174

CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

  • Upload
    others

  • View
    17

  • Download
    1

Embed Size (px)

Citation preview

Page 1: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed
Page 2: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed
Page 3: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

CHICHEWA

BIBLE CONCORDANCE

CONTRIBUTORS:Funded by: Bob and Kathy Brack

Translated to Chichewa by: Lombola Gama JuniorEdited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde

Typed and compiled by: Edwin Luciano White and Davis Galero

PROCESSED IN BLANTYRE, MALAWI

© 2004

>

All rights reserved. Permission for reproduction can only be obtained from the Foursquare Gospel ChurchNational Headquarters in Malawi or Foursquare Missions Press in Norwalk, California, USA.

Page 4: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ZA M’KATIMU

CHIPANGANO CHAKALE

Dzina Chidule Dzina Chidule

Genesis..........................................Gen Mlaliki.....................................MlalEksodo...........................................Eks Nyimbo ya Solomo..................NyimboLevitiko.........................................Lev Yesaya.....................................YesNumeri..........................................Num Yeremiya.................................YerDeuteronomo................................Deut Maliro......................................MaliYoswa..........................................Yos Ezekiele...................................EzekOweruza.......................................Owe Daniel......................................DanRute..............................................Rut Hoseya.....................................Hos1 Samuele....................................1 Sam Yowele....................................Yow2 Samuele....................................2 Sam Amosi.....................................Amo1 Mafumu....................................1 Maf Obadiya...................................Oba2 Mafumu....................................2 Maf Yona.......................................Yon1 Mbiri.........................................1 Mbi Mika........................................Mik2 Mbiri.........................................2 Mbi Nahumu...................................NahEzara............................................Eza Habakuku................................HabNehemiya.....................................Neh Zefaniya...................................ZefEstere...........................................Est Hagai.......................................HagYobu...........................................Yob Zekariya...................................ZekMasalimo....................................Mas Malaki.....................................MalMiyambo.....................................Miy

CHIPANGANO CHATSOPANO

Dzina Chidule Dzina Chidule

Mateyo.........................................Mat 2 Atesalonika ........................2 AtesMarko..........................................Marko 1 Timoteo..............................1 TimLuka.............................................Luk 2 Timoteo..............................2 TimYohane........................................Yoh Tito........................................TitMachitidwe..................................Mac Filemoni................................FileAroma..........................................Aro Ahebri....................................Aheb1 Akorinto...................................1 Akor Yakobo..................................Yak2 Akorinto..................................2 Akor 1 Petro...................................1 PetAgalatiya.....................................Agal 2 Petro...................................2 PetAefeso.........................................Aef 1 Yohane...............................1 YohAfilipi..........................................Afil 2 Yohane...............................2 YohAkolose........................................Akol 3 Yohane...............................3 Yoh1 Atesalonika..............................1 Ates Yuda......................................Yuda

Chivumbulutso......................Chiv

Za Chithunzi chomwe Chili m’Chichewa Bible Concordance:

Aimee Semple McPherson wogwiritsidwa ntchito mwamphamvu ndi Ambuye anali mu msonkhano waukulu wochitikira muhema ku California pamene UthengaWabwino wa Foursquare unauziridwa kwa iye. Anali akulankhula mau ochokera pa Ezekieli 1:1-28 pa mutu wonena kuti “Masomphenya a Ezekieli” Ezekieli anaona

chamoyo chimene ulemelero wake munthu sangathe kuulongosola. Pamene Ezekieli anapenyetsetsa pa vumbulutso la Mulungu lodabwitsali, anaona nkhope zinayi.Nkhope zinayi zimenezi Mai Pherson anazitanthauzira ndi zolinga za mabuku a Uthenga Wabwino anayi a Yesu Khristu. Pa nkhope ya Munthu, tikuona Yesu ngati

Mpulumutsi wathu, munthu wazisoni ndi wodzadza ndi kulira, akufa pamtengo. Pa nkhope ya Mkango, tikuona Yesu kuti ndi mbatizi wamphamvu wa Mzimu Woyera.Nkhope ya Ng’ombe yomwe ikuimirira wosenza katundu wolemetsa amene anasenza zofooka zathu ndi kusenza nthenda zathu zonse. Pa nkhope ya Chiombankhanga

tikuona zithunzi za Mfumu yathu ikubwera, kuchokera kumwamba kudzakwatula mkwatibwi wake.

Page 5: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MOMWE MUNGAGWIRITSIRE NTCHITO

Chichewa Bible Concordance ndi buku lomwe mungagwiritse ntchito pofuna kupeza mau ena m’Baibulo mwachangu komanso ndivesi lake. Mwachitsanzo, mwina mukufuna vesi lina lake pamene analemba kuti ‘Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimenendikulamulani’ Inu simukudziwa pomwe mau amenewa akupezeka m’Baibulo. Chomwe mungachite ndicho kusankha mau omweakupezeka mu vesi limeneli monga ‘abwenzi’ mukatero muyang’ane m,Bible Concordance mutu oti ‘abwenzi’ ndipo mukapezamuyang’anenso mau omwe akugwirizana ndi vesi limenelo.

ABWENZI (friends)abwenzi anga akundinyodola...Yob 16:20abwenzi anga anditaya...Yob 19:14wolemera amakhala ndi abwenzi ambiri...Miy 14:20nkutaya moyo wake chifukwa cha abwenzi...Yoh 15:13ndinu abwenzi anga ngati muchita...Yoh 15:14

koma ndikukutchulani abwenzi...Yoh 15:15osaletsa abwenzi ake...Mac 24:23

Pali mau ena omwe malo ena simungawapeze koma mukawapeza malo ena malingana ndi momwe awagwiritsa ntchito malingana ndimomwe aliri kuchokera m’Baibulo la Chingerezi komwe timatengera mauwa. Mwa ichi taika mau oti [onaninso] kuti muthe kupezamau amene mukufunawo malo ena. Mwachitsanzo, mau oti ‘Gulu’ lomwe mchingerezi ndi (flock) ndipo mau amenewaakumasuliridwa ndi mau osiyanasiyana. Inu muyenera kuyang’ana mau omwe akugwirizana ndi vesi lomwe mukufunalopoyang’ananso malo ena potsatira pa [onaninso:]

GULU (flock)osadya mkaka wake wa gululo...1 Akor 9:7wetani gulu la Mulungu...1 Pet 5:2okhala zitsanzo za gululo...1 Pet 5:3[onaninso:gulu la nkhosa, nkhosa, zoweta]

Chichewa Bible Concordance ilinso ndi mau amene afotokozedwa momveka kuti muthe kuwazindikira bwino. Mau ake ndi mongamaina a anthu komanso malo. Ngati dzinalo liri la anthu ambiri, pali chizindikiro cha ‘—’ chomwe chikusonyeza kuti ndi anthukapena mau osiyana. Mwachitsanzo:

NADABU (Nadab)mwana wamwamuna wamkulu pa ana anayi amuna a Aroni...Eks 6:23anatenga gawo posindikiza chipangano...Eks 24:1,9-12anakhala wansembe...Eks 28:1anaonongedwa ndi moto...Lev 10:1-7— mfumu ya Israeli...1 Maf 14:20inaphedwa ndi Basa...1Maf 15:25-31

Pamene timalemba Chichewa Bible Concordance, timagwiritsa ntchito Buku Lopatulika ndinso Buku Loyera malingana ndi momwemauwo akufotokozeredwa choncho ngati muona kuti kalembedwe kake zina zikusiyana ndi Baibulo lomwe mwatengalo, muyenerakudziwa kuti ndi Baibulo linalo.

Page 6: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

A

ARONI (Aaron)Kholo ndinso banja lake...Eks 6:16-20,23mthandizi ndi mneneri wa Mose...Eks 4:13-31;7:1,2Aonekera pamaso pa Farao...Eks 5:1-4Achita zozizwitsa...Eks 7:9,10,19,20Agwirizira manja a Mose...Eks 17:10-12Akwera phiri la Sinai; aona ulemelero wa Mulungu...Eks19:24;24:1,9,10Aweruza Israeli Mose palibe...Eks 24:14Asankhidwa ndi Mulungu kukhala wansembe...Eks 28:1Apatulidwa...Eks 29;Lev 8Ntchito yake ifotokozedwa...Eks 30:7-10Asekerera za kupembedza mafano kwa Aisraeli...Eks 32Utumiki wake wa unsembe uyambika...Lev 9Ana ake amuna apereka nsembe yachilendo ndiyosavomerezeka,kudzichepetsa kwa Aaron...Lev 10Aukira Mose...Num 12:1-16Aukiridwa ndi Kora...Num 16Apemphera kuti mliri uchoke...Num 16:45-48Ndodo yake iphuka kutsimikizira za ulamuliro wake...Num17:1Pamodzi ndi Mose, alephera ku Meriba...Num 20:1-13Amwalira, mwana wake alowa m’malo mwake mongawansembe...Num 20:23-29unsembe wake ufanizidwa ndi:unsembe wa Melikizedeki...Aheb 7:11-19unsembe wa Khristu...Aheb 9:6-15,23-28

ABAALA (Baals)milungu ya a Kanani...Ower 10:10-14anagwira Israeli mwa ndale...Ower 2:11-14;3:7Ahazi apangira mafano...2 Mbir 28:1-4

ABADONI (Abddon)mngelo wolamulira chiphompho chija...Chiv 9:11

ABALE (brethren)pamaso pa abale ake onse...Gen 16:12usandikuze pa abale ako...Deut 17:20ndipo inu nonse muli abale...Mat 23:8munachitira ichi m’modzi wa abale...Mat 25:40pitani, kauzeni abale anga...Mat 28:10mwana woyamba wa abale...Aro 8:29kuweruza pa abale...1 Akor 6:5koma pa kuchimwira abale...1 Akor 8:12abale oposa mazana asanu...1 Akor 15:6moopsa mwa abale onyenga...2 Akor 11:26abale onyenga olowezedwa m’tseri...Agal 2:4kufanizidwa ndi abale m’zonse...Aheb 2:17mukakonde abale ndi chikondi chosanyenga...1 Pet 1:22chifukwa tikondana ndi abale...1 Yoh 3:14moyo wathu chifukwa cha abale...1 Yoh 3:16salandira abale iye yekha...3 Yoh 10wa abale ako aneneri...Chiv 22:9[onaninso Mbale, Chibale, Chapaabale]

ABALE (brotherhood)kondani abale...1 Pet 2:17zirimkukwaniridwa pa abale...1 Pet 5:9

ABALE (brotherly)chikondi cha pa abale...Aheb 13:1

ABALE (brothers)abale anga anachita monyenga ...Yob 6:15abale anga adandiyesa mlendo...Mas. 69:8amai anga ndi abale anga ...Marko 3:33

amai anga ndi abale anga...Luk 8:21angakhale abale ake...Yoh 7:5okondana ndi abale...1 Pet 3:8

ABBA (Abba)Abba, Atate, zinthu zonse...Marko 14:36umene tifuula nao kuti Abba, Atate...Aro 8:15wofuula Abba, Atate…Agal 4:6

ABEDINEGO (Abed-nego)dzina lopatsidwa Azariya, kapolo wachihebri…Dan 1:7wasankhidwa ndi Nebukadinezara ...Dan 2:49anakana kupembedza mafano naponyedwa m’ng’anjo yamoto,anaomboledwa...Dan 3:12-30

ABELE-BETI-MAAKA (Bel-beth-maachah)unagonjetsedwa ndi Tigilati pileseke…2 Maf 15:29Kothawirako kwa Sheba, opulumutsidwa kuchionongeko...2Sam 20:14-22wongonjetsedwa ndi Benihadadi...1 Maf 15:20

ABELE (Abel)mwana wachiwiri wa Adamu...Gen 4:2nsembe yake inavomerezedwa ndi Mulungu…Gen 4:4anaphedwa ndi Kaini...Gen 4:8nsembe yake inaperekedwa mwa chikhulupiriro…Aheb 11:4

ABIEZIRI (Abiezrites)abale ake a Gideoni...Ower 6:11,24,34

ABIGAYELI (Abigail)mkazi wa nzeru wa Nabala wopusa …1 Sam 25:3anasangalatsa Davide ndipo anakhala mkazi wake...1 Sam25:14-42mayi wake wa Kileabu ...2 Sam 3:3

ABIHU (Abihu)mwana wamwamuna wachiwiri wa Aaroni...Eks6:23apereka nsembe ya moto wachilendo ndi amwalira...Lev 10:1-

7

ABIMELEKE (Abimelech)mfumu ya ku Gerari, idatenga Sara mosadziwa …Gen 20:1-18adapangana pangano ndi Abrahamu …Gen 21:22-34— Mfumu yachiwiri ya Gerari, idamthamangitsa Isake...Gen26:1-6adapanga pangano ndi Isake...Gen 26:17-33— mwana wa Gideoni kudzera mwa Mzikazi wake…Ower8:3anapanga chiwembu kuti akhale mfumu…Ower 9

ABINADABU (Abinadab)munthu wa ku Kiriati-yeari amene mnyumba yakemumasungidwa likasa...1 Sam 7:1,2— mwana wamwamuna wachiwiri kwa ana asanu ndi awiri aJese ...1 Sam 16:8anatumikira mgulu la nkhondo la Saulo… Sam 17:13— mwana wamwamuna wa Saulo amene anaphedwa paGiliboa...1 Sam 31:1-8amene mafupa awo anaikidwa ndi amuna aku Yabesi...1 Mbir10:1-12

ABINERI (Abner)kazembe wa khamu la ankhondo, mbale wa bambo a Saulo...1Sam 14:50,51anadzudzulidwa ndi Davide...1 Sam 26:5,14-16anamthandizira Isiboseti; anagonjetsedwa ndi a nkhondo aDavide,anapha Asahele...2 Sam 2:8-32anapangana ndi Davide...2 Sam 3:6-21

Page 7: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

anaphedwa ndi Yowabu, naliridwa ndi Davide...2 Sam3:22-39

ABIRAMU (Abiram)mwana wa fuko la Rubeni yemwe anaukira Mose... Num16:1-50

ABISAGI (Abishag)waku Sunamu wotumikira ndi kusamala mfumu...1 Maf1:1-4,15anachitira umboni za kusankhidwa kwa Solomoni kukhalamfumu 1 Maf 1:15-31Adoniya anaphedwa chifukwa chokhumbira kukwatira iye...1Maf 2:13-25

ABISAI (Abishai)mdzukulu wa Davide, anagwirizana ndi Yoabu pobwezeraAbineri...2 Sam 2:18-24womvera kwa Davide pamene Abisalomu ndi Sebaankadzudzulidwa,2 Sam 16:9-12;19:21-23anadzudzulidwa ndi Davide...2 Sam 16:9-12;19:21-23Zazikulu zimene anachita...2 Sam 21:16-17; 23:18; 1 Mbir18:12-13

ABISALOMU (Absalom)mwana wamwamuna wa Davide...2 Sam 3:3anapha Amnoni chifukwa chogwirira Tamara, nathawa...2

Sam 13:20-39anabwerera kudzera mwa Yoabu ndipo anayanjanitsidwa ndi

Davide…1 Sam 14anafuna kulanda mpando waufumu mwaupandu...2 Sam

15:1-18;8anagwidwa ndi kuphedwa ndi Yoabu…2 Sam 18:9-18analiridwa ndi Davide...2 Sam 18:19; 19:8

ABIYA (Abijah)mwana wamwamuna wachiwiri wa Samuele, anatsatira njirazachinyengo…1 Sam 8:2,3— Mbeu ya Aroni, wamkulu pa ntchito ya ansembe...1 Mbir24:3,10Zakariya anali wagulu la ansembe la Abiya…Luk 1:5— mwana wa Yerobiamu...1 Maf 14:1-18— dzina lina la mfumu Abiyamu...2 Mbir 11:20mfumu ya a Yuda...1 Maf 14:31anatsatira machimo a atate ake...1 Maf 15:1-7anagonjetsa Yerobiamu ndi kutenga mizinda...2 Mbir13:13-20

ABIYATARA (Abiathar)wansembe yemwe anamthawa Saulo ku Nobu...1 Sam22:20-23anakhala wansembe wamkulu pansi pa ulamuliro waDavide...1 Sam 23:6,9-12anakhala okhulupirika kwa Davide…2 Sam 15:24-29anadziwitsa mfumu Davide za Ahitofele...2 Sam 15:34-36adachotsedwa pa ntchito ya unsembe ndi Solomoni...1 Maf2:26,27,35adavomereza kuwukira kwa Adoniya...1 Maf 1:7,9,25

ABRAHAMU (Abraham, Abram)mndandanda wa anthu ndi mabanja (maanja) kapenamakolo...Gen 11:26-31analandira maitanidwe kuchokera kwa Mulungu, nalowam’Kanani ...Gen 12:1-6Mulungu anamulonjeza dziko la Kanani, anamanga hemakufupi ndi Beteli…Gen 12:7,8anawanamiza Aigupto zokhuza Sarai…Gen 12:11-20analekana ndi Loti, analandira Kanani…Gen 13anapulumutsa Loti ku ukapolo...Gen 14:11-16anapereka chakhumi kwa Melikizedeke, anakana zinthuzolandidwazo...Gen 14:18-24

lonjezo linapangidwa latsopano, analonjezedwamwana wamwamuna...Gen 15anatenga Hagara ngati mzikazi, Ismayeli anabadwa…Gen 16dzina lake linasinthidwa kuchokera ku Abramu, analamulidwamdulidwe...Gen 17analandira Ambuye ndi Angelo...Gen 18:1-15anapembedzera Sodomu...Gen 18:16-33anamnamiza Abimileke zokhuza Sara…Gen 20kubadwa kwa Isake...Gen 21:1-7anathamangitsa Hagara ndi Ismaeli...Gen 21:9-14anapereka Isake nsembe pomvera Mulungu...Gen 22:1-19anampezera Isake mkazi...Gen 25:1-10anakwatira Ketura; nalera ana ena; nafa...Gen 25:1-10mnzake wa Mulungu...2 Mbir 20:7wolungamitsidwa mwa chikhulupiriro…Aro 4:1-12tate kapena bambo wa okhulupirira enieni...Aro 4:11-25ali mu ndandanda ya anthu achikhulupiriro...Aheb 11:8-10kwawo kwa muyaya, kumwamba...Luk 16:19-25

ABULU (donkeys)okwera pa abulu ndi...Yes 21:7[onaninso: mbidzi]

ABUSA (pastors)ena alaliki, ena abusa ...Aef 4:11

ABUSA (shepherds)adzakhala abusa...Num 14:33abusa nawonso ndi...Yes 56:11ndipo ndidzakupatsani abusa...Yer 3:15abusa amene amaononga...Yer 23:1abusa amene adyetsa anthu anga...Yer 23:2abusa ao anawasokoneza...Yer 50:6abusawo adadzidyetsa okha...Ezek 34:8panali abusa m’dziko lomwelo... Luk 2:8

ABWENZI (friends)abwenzi anga akundinyodola...Yob 16:20abwenzi anga anditaya...Yob 19:14wolemera amakhala ndi abwenzi ambiri...Miy 14:20nkutaya moyo wake chifukwa cha abwenzi...Yoh 15:13ndinu abwenzi anga ngati muchita...Yoh 15:14koma ndikukutchulani abwenzi...Yoh 15:15osaletsa abwenzi ake...Mac 24:23

ACHIBWIBWI (stammerers)achibwibwi adzalankhula...Yes 32:4

ACHIGOLOLO (adulterers)ladzala ndi a chigololo...Yer 23:10kapena a chigololo...1 Akor 6:9adama ndi a chigololo...Aheb 13:4akazi a chigololo...Yak 4:4

ACHINYENGO (deceitful)okhetsa mwazi ndi achinyengo ...Mas 55:23uphungu wa oipa unyenga...Miy 12:5

ACHIPHAMASO (hypocrites)monga anthu achiphamaso...Mat 6:5anthu achiphamasonu...Mat 22:18Afarisi, anthu achiphamaso...Mat 23:13sindiyenda ndi anthu achiphamaso...Mas 26:4[onaninso: onyenga]

ACHULE (frogs)ndidzalilanga polidzaza ndi achule...Eks 8:2mizimu yonyansa yonga achule...Chiv 16:13

ADAMA (fornicators)anthu adama ndi a chigololo...Aheb 13:4

Page 8: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ADAMU (Adam)kulengedwa kwake...Gen 1:26,27;2:7apatsidwa ulamuliro wolamulira dziko lonse lapansi...Gen1:28-30apatsidwa mkazi...Gen 2:18-25Kuyesedwa, kugwa ndi kuchotsedwa m’munda waEdeni...Gen 3Ana ake...Gen 4:1,2;5:3,4kusamvera kwake kunabweretsa tchimo ndi imfa...Aro 5:12-14— Adamu wotsiriza ndinso wachiwiri, yemwe ndiKhristu...Aro 5:14,15;1 Akor 15:20-24,45-48

ADANI (adversaries)adzatswanya adani ake...1 Sam 2:10ndidzawatha adani anga...Yes 1:24zimene adani anuwo...Luk 21:15ndiponso adani alipo...1 Akor 16: 9osalola kuti adani anu...Afil 1:28[onaninso: otsutsana, vuta]

ADANI (enemies)Chauta muwamwaze adani anu...Num. 10:35adandipulumutsa kwa adani anga...Mas 18:48chakudya adani anga akuwona...Mas 23:5musalole kuti adani anga andichititse manyazi...Mas 25:2ngamphamvu adani amene amafuna moyo wanga...Mas 38:19mitu ya adani ake...Mas 68:21adani ake adzadya fumbi...Mas 72:9wanzeru kuposa adani anga...Mas 119:98ndimawayesa adani anga...Mas 139:22muzikonda adani anu...Mat 5:44adani a munthu adzakhala am’banja...Mat 10:36adzatipulumutsa kwa adani athu...Luk 1:71ife tinali adani a Mulungu...Aro 5:10Ayuda asanduka adani a Mulungu...Aro 11:28mpaka atagonjetsa adani ake onse...1 Akor 15:25okhala alendo kale ndi adani...Akol 1:21Mulungu asandutse adani ake...Aheb 10:13kukamwa kwao kuononga adani...Chiv 11:5

ADANI (foe)akundisautsa ndi adani anga...Mas 27:2nabalalitsa adani ake...Mas 18:14

ADANI (foes)akundisautsa ndi adani anga...Mas 27:2ndidzatswanya adani ake...Mas 89:23

ADONI-ZEDEKI (Adoni-zedek)Mfumu ya ku Yerusalemu...Yos 10:1-5Anagonjetsedwa ndi kuphedwa ndi Yoswa...Yos 10:6-27

ADONIYA (Adonijah)Mwana wamwamuna wa chinayi wa Davide...2 Sam 3:2,4Anafuna kulanda ufumu mwaupandu...1 Maf 1:5-53Anakhumbira Abisagi kukhala mkazi wake...1 Maf 2:13-38Anachotsedwa ndi Solomoni...1Maf 2:19-25

ADORAMU (Adoniram/Adoram)wamkulu pansi pa Davide, Solomoni ndi Rehobowamu Sam20: 24, 1 Maf 5: 14, 12: 18anaponyedwa miyala ndi a Israeli olusa...1 Maf 12:18wotchedwa Hadoramu...2 Mbir 10: 18

ADZAKAZI (maidservants)adzakazi ake alira ngati mau ...Nah 2:7pa akapolo anga ndi adzakazi...Mac 2:18

AEDOMU (Edomites)zidzukulu za Esau...Gen 36:9

anakaniza Aisraeli kudutsa...Num 20:18-20mdani kwa Israeli...Gen 27:40;1 Sam 14:47;2 Mbir20:10;Mas 137:7ananeneredwa uneneri...Gen 27:37;Yes 34:5-17;Ezek25:12-14;35:5-7;Amo9:11,12

AEPIKUREA (Epicureans)gulu la anthu anzeru...Mac 17:18

AETIOPIYA (Ethiopians)khungu lawo, losasintha...Yer 13:23

AFEKI (Aphek)mzinda ku chigwa cha Saroni...Yos 12: 18dera lomwe Afilisti anamanga zithando kapena zigonozawo...1 Sam 4:1;29:1— mzinda wa mu Yezereli...1 Maf 20:26-30kugwa kwa Asiriya kunaneneredwa pa malo amenewa...2 Maf13:14-19

AFILISTI (Philistines)sanagonjetsedwe kapena kuthiridwa nkhondo ndi Yoswa...Yos13:1-3anasiyidwa kuti akayese Israeli...Ower 3:1-4Mulungu anapereka Israeli m’manja mwao mongachilango...Ower 10:6,7Israeli anaomboledwa kuchokera kwa iwo ndi Samson...Ower13-16analanda, ndi kubweza likasa la Mulungu...1 Sam 4-6anamenya nkhondo ndi Saulo ndi Davide...1 Sam13:15-14:23;17:1-52;18:25-27;21:10-15;27:1-28:6;29:1-11;31:1-13;2 Sam 5:17-25poyambirira anali pa chilumba cha Kafita...Yer 47:4

AGAGI (Agag)mfumu ya Ameleke nthawi ya uneneri wa Balamu…Num 24:7— mfumu ya Ameleke, inasungidwa ndi Saulo, inaphedwa ndiSamuele1Sam 15:8,9,20-24,32,33

AGALILEYA (Galileans)Pilato adaalamula kuti aphedwe..Luk 13:1,2

AGALU (dogs)ali ngati agalu anjala...Yes 56:11musamapatsa agalu zinthu zopatulika...Mat 7:6ngakhale agalu omwe amadyako nyenyeswa...Mat15:27ngakhale agalu ankabwera...Luk 16:21kunja kuli agalu ndi anyanga...Chiv 22:15

AGERASA (Gergesenes)Achiritsa ogwidwa ndi ziwanda...Mat 8:28-34anthu akum’mawa kwa nyanja ya Galileya...Marko 5:1

AGRIKI (Greeks)anthu a ku Grisi...Yow 3:6;Mac 16:1mzinda wa uzimu...Aro 10:12ena anakhulupirira...Mac 14:1

AGWA (ensnared)iwo onse agwa m’mauna...Yes 42:22[onaninso: kodwa]

AHABU (Ahab)mfumu yosamvera ya Israeli...1 Maf 16:29anakwatira Yezebeli nalimbikitsa kupembedza baala...1 Maf16:31-33;18:17-46sanagwirizane ndi Eliya...1 Maf 17:1anamenya nkhondo ndi Benidadi...1 Maf 20:1-43anakhumbira kwambiri munda wa mpesa wa Naboti...1 Maf21:1-16imfa yake inaneneredwa, kulapa kwake kunachedwetsa

Page 9: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

chiweruzo...1 Maf 21:17-29anapita kunkhondo ngakhale Mikaya anachenjeza kutiasapite...1 Maf 22:1-37uneneri umene unaneneredwa pa iye unakwaniritsidwa...1 Maf22:38— mneneri wabodza...Yer 29:21-23

AHASWERO (Ahasuerus)tate a Dariyo, mbewu ya Amedi... Dan 9:1— mfumu ya Perisiya...Ezara 4:6, Est 1:1inampanga Estere kukhala mkazi wake...Est 2:16,17analamulira kuti Ayuda awonongedwe malinga ndi uphunguwa Hamani...Est 3:8-15anasintha lamulo lake lopha Ayuda chifukwa cha pempho laEstere...Est 10:1-3

AHAZI (Ahaz)mfumu ya Ayuda, anagwiritsa ntchito Kachisi pazodetsedwa...2 Maf 16anagonjetsedwa ndi Siriya ndi Israeli...2 Mbir 28:5-15analimbikitsidwa ndi Yesaya, anakana kupemphachizindikiro...Yes 7:1-17

AHAZIYA (Ahaziah)mfumu ya Israeli; mwana wa Ahabu ndi Yezebeli,wopembedza Baala...1 Maf 22: 51-53anagwera pa zitsonga, Zebubu, anafa monga mwa mau aEliya...2 Maf 1:2-18— mfumu ya Yuda; analamulira moyipa...2 Maf 8:25-29;2Mbir 22:1-60Anaphedwa ndi Yehu...2 Maf 9:27-29;2 Mbir 22:7-9

AHELENESTE (Hellenists)Ayuda oyankhula Chigiriki...Mac 6:1anamukana Paulo...Mac 9:29uthenga wabwino unalalikidwa kwa iwo...Mac 11:20

AHERODE (Herodians)anakhalira limodzi ndi Afarisi potsutsana ndi Yesu...Marko3:6anafuna kumkola Yesu...Mat 22:15-22anachenjeza anthu za iwo...Marko 8:15

AHIKAMU (Ahikam)anatumizidwa kwa Hulida...2 Maf 22:12-14anamteteza Yeremiya...Yer 26: 24tate wa Gedaliya, wolamulira pansi pa Nebuchadinezara...2Maf 25:22;Yer 39:14

AHIMAAZI (Ahimaaz)mwana wa Zadoki mkulu wansembe...1 Mbir 6:8,9anamchenjeza Davide za zolinga za Abisalomu …2 Sam15:27,36woyamba kumuuza Davide za kugonjetsedwa kwaAbisalomu...2 Sam 18: 19-30

AHIMELEKI (Ahimelech)wamkulu wa ansembe nthawi ya ulamuliro wa Saulo...1 Sam21:1-9anaphedwa ndi Doegi, m’modzi mwa ana ake amuna,Abiyatala anathawa...1 Sam 22:9-20Davide akukamba za iye...Mas 52

AHINOAMU (Ahinoam)mkazi wa Davide...1 Sam 25:43;27:3;30:5,18amake a Amnoni...2 Sam 3:2

AHITI (Hittites)limodzi la maiko asanu ndi awiri aku Kanani...Deut 7:1Aisraeli anakwatiwa ndi kukwatirana nawo...Ower 3:5,6;1Maf 11:1;Ezara 9:1,2

AHITOFELI (Ahithophel)mphungu wa Davide...2 Sam 15-12analowa chiwembu cha Abisalomu ndi kumpatsa Abisalomuuphungu...2 Sam 15:31;16:20-23uphungu wake unakanidwa, anadzipha yekha...2 Sam 17:1-23

AHIVI (Hivites)limodzi la maiko asanu ndi awiri aku Kanani...Deut 7:1Esau anakwatira nao...Gen 36:2Agibeoni anali ochokera ku fuko limeneli...Yos 9:3,7

AHIYA (Ahijah)mneneri wa ku Silo yemwe ananenera kugawanika kwa ufumuwa Solomoni...1Maf 11:29-39ananenera kuchotsedwa ndi kugwa kwa Yerobiamu...1Maf14:1-18mlembi wa uneneri...2 Mbir 9:29

AHORI (Horites)anthu okhala ku phiri la Seiri...Gen 36:20anagonjetsedwa ndi Kedorilaomere...Gen 14:5,6anachotsedwa ndi zidzukulu za Esau...Gen 36:20-29;Deut2:12,22

AISMAELE (Ishmaelites)anakhala ku Havila...Gen 25:17,18Yosefe anagulitsidwa kwa iwo...Gen 37:25-28anagulitsa Yosefe kwa Potifara...Gen 39:1

AISRAELI (Israelites)anazungulira mu chipululu...Num 14:26-39anaoloka Yordane; anagonjetsa Kanani...Yos 4;12analamuliridwa ndi Oweruza...Ower 2Saulo anasankhidwa kukhala mfumu...1 Sam 10ufumu unagawika...1 Maf 12ufumu wakumpoto unatengedwa ukapolo...2 Maf 17ufumu wakummwera unatengedwa ukapolo...2 Maf 24anakhala zaka 70 ku ukapolo...2 Mbir 36:20,21kubwerera utatha ukapolo...Ezara 1:1-5fuko lokana Khristu...Mat 27:20-27dziko loonongedwa...Luk 21:20-24anazunzidwa ku Ejipito...Eks 1:12-22anachoka ku Ejipito...Eks 12:29-42,50;13:17-22analandira malamulo ku Sinai...Eks 19amapembedza mafano ndi kuukira...Eks 32;Num 13;14

AKALONGA (princes)wosasamalira nkhope za akalonga...Yob 34:19ndipo akalonga ako adyera mamawa...Mlal 10:16ndipo akalonga ako adya pa nthawi yoyenera...Mlal 10:17ndi akalonga adzalamulira m’chiweruzo...Yes 32:1amene asandutsa akalonga kuti akhale achabe...Yes 40:23[onaninso: akuru, nduna]

AKANANI (Canaanites)Aisraeli analamulidwa kuwachotsa pakati pawo ndipoasatumikire milungu yawo,Eks 23:23-33anachotsa chidani chawo...Lev 18:24-30Aisraeli anauzidwa kuti asapangane nawo ndipo asakwatiranenawo...Deut 7:1-3

AKANI/AKARA (Achan/Achar)tchimo lake linabweretsa kulephera kwa Aisraeli...Yos 7:1-15anaphedwa poponyedwa miyala...Yos 7:16-25tchimo lake linakumbukiridwa...Yos 22:20wotchedwanso Akara...1 Mbir 2:7

AKAPOLO (bondservants)akapolo inu mverani ambuye anu...Aef 6:5Ambuye inu, chitirani akapolo...Akol 4:1koma ngati akapolo a Mulungu...1Pet 2:16

Page 10: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

AKAPOLO (menservants)ngakhale pa akapolo anga...Yos 2:29ngakhale mwa akapolo anga...Mac 2:18

AKAPOLO (servants)ndaona akapolo akuyenda...Mlal 10:7akutilamulira ndi akapolo...Mali 5:8[onaninso: atumiki]

AKAPOLO (slaves)tisakhalenso akapolo...Aro 6:6kale munali akapolo...Aro 6:17akapolo a zonyansa...Aro 6:19musasanduke akapolo...1 Akor 7:23

AKASIDI (Chaldeans)anamchitira nkhondo Yobu...Yob 1:17Nebukadinezara, mfumu ya a Kasidi...2 Maf 25:1-21Babulo, ulemerero wa a Kasidi...Yes 13:19ananeneredwa kuti adzatenga a Yuda ukapolo...Yer 25:1-26anali kugwiritsidwa ntchito ndi Mulungu...Hab 1:6

AKASUPE (fountains)akasupe onse a madzi akulu amasefukira...Gen 7:11ndipo anatsekedwa akasupe a madzi aakulu...Gen 8:2dziko la mitsinje ya madzi, la akasupe...Deut 8:7ndi madzi oyenda a m’kasupe mwako...Miy 5:16pamene panalibe akasupe odzala madzi...Miy 8:24pokula akasupe a zozama...Miy 8:28pazitunda zoti se, ndi akasupe pakati pa zigwa...Yes 41:18nadzawatsogolera ku akasupe a madzi...Chiv 7:17

AKASUPE (springs)mumatumphutsa akasupe...Mas 104:10lidzasanduka la akasupe...Yes 35:7akasupe adzatumphuka...Yes 41:18ngakhale pa akasupe wa madzi adzawachotsera...Yes 49:10mtunda ndi nyanja ndi akasupe amadzi...Chiv 14:7anatsanulira mbale yake ku mitsinje ndi akasupeamadzi...Chiv 16:4

AKATSWIRI A MALAMULO (lawyers)Afarisi ndi akatswiri amalamulo...Luk 7:30muli ndi tsokanso, inu akatswiri amalamulo...Luk 11:46

AKATUNDU (burdens)napenya akatundu awo...Eks 2:11amanga akatundu olemera...Mat 23:4musenzetsa anthu akatundu osautsa ponyamula...Luk 11:46inu nomwe simukhudza akatunduwo ndi chala...Luk 11:46

AKAVALO (horses)akapolo akuyenda pa akavalo...Mlal 10:7akavalo ao ngaliwiro kuposa...Yer 4:13pa thanthwe akavalo nkuthamanga...Amo 6:12ngati tiikira akavalo zogwirira mkamwa...Yak 3:3

AKAYA (Achaia)Mzinda umene Paulo anachezera...Mac 18:1,12Apolo analalikiramo...Mac 18:24-28Uthenga Wabwino unalalikidwa monsemo...1 Ates 1:7,8

AKAZI (women)wodala ndi iye kupambana akazi onse...Ower 5:24ana aakazi a mafumu...Mas 45:9wokongola kuposa akazi...Nyim 1:8akukulamulani ndi akazi...Yes 3:12akazi akhale chete...1 Akor 14:34kuti akalangize akazi aang’ono akonde amuna awo...Tit 2:4akazi oyera mtima akuyembekezera Mulungu...1 Pet 3:5

amene sadetsedwa pamodzi ndi akazi...Chiv 14:4

AKAZI A MASIYE (widows)akazi amasiye ndinkawasangalatsa...Yob 29:13mtetezi wa azimai amasiye...Mas 68:5akazi anu amasiye akhoza...Yer 49:11azimai amasiye a zaka...1 Tim 5:14ana amasiye ndi akazi amasiye...Yak 1:27

AKAZI ADAMA (harlots)paja pamasamba akazi adama...1 Maf 22:38akazi adama akulowa mu...Mat 21:31

AKERUBI (Cherubim)Mulungu adaika a Kerubi...Gen. 3: 24)amene mukhala pa a Kerubi...Mas 80:1makala oyaka amene ali pakati pa a Kerubi...Ezek 10:2panali zithunzi za a Kerubi...Aheb 9:5

AKHATE (lepers)pofika akhate ao...2 Maf 7:8munali akhate ambiri mu Israeli...Luk 4:27

AKHRISTU (Christians)Kumene ophunzira adayamba kutchedwa Akhristu...Mac11:26

AKHRISTU (Christs)chifukwa akhristu onama adzauka...Mat 24:24

AKHUNGU (blind)ndinali maso a akhungu...Yob 29:15ndikukhala akhungu...Yes 29:9kuti atsegule maso akhungu...Yes 42:16ndipo ndidzayendetsa akhungu...Yes 43:8turutsani anthu akhungu...Yes 56:10asokela m’makwalala ngati akhungu...Mali 4:14akhungu alandira kuona...Mat 11:5ali atsogoleri akhungu...Mat 15:14ndi akhungu kuti apenyenso...Luk 4:18[onaninso: khungu, wakhungu]

AKISA (Achsah)mwana wamkazi wa Kalebi...1 Mbir 2:49anampereka kwa Otiniyeli...Yos 15:16-19anapatsidwa zitsime za madzi...Ower 1:12-15

AKISI (Achish)mfumu ya ku Gati...1 Sam 21:10-15kumene Davide anathawira...1 Sam 27:1-12anaumirizidwa kuti amchotse Davide...1 Sam 29:1-11analanda akapolo awiri a Simeyi...1 Maf 2:39,40

AKORI/CHIGWA CHA AKORI (Achor, valley of)malo amene anagendera Akani...Yos 7:24-26anali malire aYuda...Yos 15:7okhuza malonjezano...Yes 65:10

AKORONA (crowns)pamitu pao akorona agolide...Chiv 4:4[onaninso: nduwira zachifumu]

AKUBA (robbers)Israeli kwa anthu akuba...Yes 42:24ndisanafike, ngakuba ndi olakwa...Yoh 10:8

AKUBADWA (generation)akubadwa oipa achigololo...Mat 12:39[onaninso: akubadwa, mibadwo, mbadwo]

AKUFA (dead)tiri akufa tonse...Eks 12:33

Page 11: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

anaima pakati pa akufa...Num 16:48mudzachitira akufa zodabwitsa...Mas 88:10monga iwo adafa kale lomwe...Mas 143:3koma akufa sadziwa kanthu...Mlal 9:5akufa anu adzakhala ndi moyo...Yes 26:19akufa aike akufa ao...Mat 8:22ndi akufa akuukitsidwa...Mat 11:5sali Mulungu wa akufa...Mat 22:32mwana wanga uyu anali wakufa...Luk 15:24akufa adzamva mau a Mulungu...Yoh 5:25Khristu anaukitsidwa kwa akufa...Aro 6:4mudziwerengere inu nokha ofafa...Aro 6:11popanda lamulo uchimo uli wakufa...Aro 7:8Ambuye wa akufa ndi wa amoyo...Aro 14:9kuti waukitsidwa kwa akufa...1 Akor 15:12amene abatizidwa chifukwa cha akufa...1 Akor 15:29pokhala munali akufa ndi zolakwa...Aef 2:1akufa mwa Ambuye adzayamba kuuka...1 Ates 4:16adafa pokhala ali ndi moyo...1 Tim 5:6chikhulupiriro chopanda ntchito chili chakufa...Yak 2:26otsala a akufa...Chiv 20:5ndipo ndinaona akufa...Chiv 20:12

AKULA (Aquila)amene anamulandira Paulo ku Korinto...Mac 18:2,3anapita ku Siriya ndi ku Efeso pamodzi ndi Paulo...Mac18:18,19anamulangiza Apolo...Mac 18:24-26analemekezedwa ndi kukhumbiridwa ndi Paulo...Aro 16:3,4

AKULU (elders)akulu a Israyeli...Eks 24:1kuwaphunzitsa nzeru akulu-akulu...Mas 105:22akuluakulu sadzakhalanso ndi uphungu...Ezek 7:26ndi kukanidwa ndi akuru ndi ansembe akuru...Luk 9:22adakhazika akulu ampingo...Mac 14:23kuitana akulu ampingo...Mac 20:17akulu ampingo otsogolera mpingo...1 Tim 5:17kuti uike akulu ampingo mu mzinda...Tit 1:5pakuti momwemo akulu adachitidwa umboni...Aheb 11:2aitanitse akulu ampingo...Yak 5:14akulu ampingo amene ali pakati panu...1 Pet 5:1pamipandopo padakhala akuluakulu...Chiv 4:4

AKULU AMILANDU (councils)adzakuperekani kwa akulu amilandu...Marko 13:9

AKUNJA (Gentiles)anthu akunja azifunitsa zonsezi...Mat 6:32[onaninso: amitundu]

AKURU (princes)kuti amkhalitse pamodzi ndi akuru...Mas 113:8koposa kukhulupirira akuru...Mas 118:9ngakhale kukwapula akuru...Miy 17:26ndipo ndidzapereka ana kuti akhale akuru ao...Yes 3:4[onaninso: akalonga, nduna]

ALALIKI (evangelists)ena aneneri, ena alaliki...Aef 4:11

ALENDO (aliens)pakuti ndakonda alendo...Yer 2:25alendo anatha...Hos 7:9alendo apadera...Aef 2:12ankhondo yachilendo...Aheb 11:34

ALENDO (foreigners)alendo adzamanganso malinga...Yes 60:10ndi alendo okhala kumeneko...Mac 17:21sindinunso alendo kapena akudza...Aef 2:19

ALENDO (strangers)zidzakhala alendo...Gen 15:13alendo afunkhe...Mas 109:11Chauta amateteza alendo...Mas 146:9alendo akukuwonongerani...Yes 1:7“anthu achilendo...”...Yes 61:5sizidziwa mau a alendo...Yoh 10:5Khristu munali alendo...Aef 2:12ngati walera ana, ngati wachereza alendo...1 Tim 5:10sindinunso alendo...Aheb 11:13kumalandira bwino alendo...Aheb 13:2makamaka akakhala alendo...3 Yoh 5

ALEVI (Levites)anapatsidwa mphoto chifukwa chodzipereka...Eks 4:14anasankhidwa kuyang’anira hema...Num 1:47-54analowetsedwa m’malo mwa ana oyamba a Israeli...Num3:12-45anayeretsedwa ku ntchito ya Ambuye...Num 8:5:26mizinda inapatsidwa kwa iwo...Num 35:2-8;Yosw14:3;1 Mbir6:54:81anaikidwa kukagwira ntchito ya mkachisi...1 Mbir9:14-34;23:1-26:28

ALIYENSE (everyone)aliyense mwa inu akaleka makhalidwe...Yer 25:5aliyense amene abadwa mwa Mzimu Woyera...Yoh 3:8aliyense wokonda choona...Yoh 18:37

ALONDA (watchmen)alonda adandipeza...Nyi 3:3alonda anu akweza...Yes 52:8alonda ache ali akhungu...Yes 56:10ndaikapo alonda...Yes 62:6Chauta adakupatsani alonda...Yer 6:17muike alonda...Yer 51:12

AM’NDENDE (captive)mutatenga am’ndende ambiri...Mas 68:18adzatengedwa ndende...Amo6:7nadzagwidwa ndende...Luk 21:24adatenga chigulu cha am’ndende...Aef 4:8

AMALIWONGO (foes)pamene adani ndi amaliwongo anga...Mas 27:2

AMANGAWA (debtors)monga ifenso takhululukira amangawa...Mat 6:12amangawa onse a mbuye wake...Luk 16:5ife tiri amangawa...Aro 8:12ndiponso iwo ali amangawa awo...Aro15:27

AMANTHA (cowardily)koma amantha ndi osakhulupirira...Chiv 21:8

AMASIYE (fatherless)ndidaopsezapo mwana wamasiye...Yob 31:21wamasiye mukhala mthandizi...Mas 10:14mudzawateteza amasiye...Mas 10:18ndiponso mwana wamasiye...Mas 146:9minda ya ana amasiye...Miy 23:10satchinjiriza ana amasiye...Yes 1:23amafunkha za akazi amasiye...Yes 10:2mumachitira chifundo amasiye...Hos 14:3

AMATSENGA (charmers)liwu loitana la kamatsenga...Mas 58:5

AMBUYE (LORD)usamuyese Ambuye Mulungu...Mat 4:7Ambuye Mulungu wako udzigwadira...Mat 4:10amene ali Khristu Ambuye...Luk 2:11

Page 12: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

munditchuliranji ine Ambuye, Ambuye...Luk 6:46nanena, Ambuye anauka ndithu...Luk 24:34ine mphunzitsi ndi Ambuye...Yoh 13:13Yesu Khristu ndiye Ambuye wa onse...Mac 10:36ndinati, ndinu yani Ambuye...Mac 26:15m’kati mwako Yesu ndiye Ambuye...Aro 10:9pakuti yemweyo ali Ambuye wa...Aro 10:12akhoza kunena Yesu ali Ambuye...1 Akor 12:3Ambuye ndiye Mzimuyo...2 Akor 3:17kuti Yesu Khristu ali Ambuye...Afil 2:11ndi Ambuye wathu Yesu Khristu...Yuda 4ufumu Ambuye Mulungu wathu...Chiv 19:6[onaninso: Yehova]

AMBUYE (lords)iriko milungu yambiri ndi ambuye...1 Akor 8:5chifukwa ali Mbuye wa ambuye...Chiv 17:14

AMBUYE (masters)ambuye ena adatilamuira ife...Yes 26:13kukhala kapolo wa ambuye awiri...Luk 16:13Ambuye inu chitirani akapolo...Akol 4:1akukhala nao ambuye okhulupirira...1Tim 6:2

AMIDIYANI (Midianites)zidzukulu za Abrahamu kudzera mwa Ketura...Gen 25:1,2Mose anathawirako...Eks 2:15anatsatira Moabu potemberera Israeli...Num 22:4-7anakwatirana ndi anthu omwe Mulungu anawakwiyira...Num25:1-18anagonjetsedwa ndi Israeli...Num 31:1-10anazunza Israeli; anagonjetsedwa ndi Gidioni...Ower 6;7

AMITUNDU (gentiles)anagawa zisi za amitundu m’maiko mwao...Gen 10:5kuwala kounika anthu amitundu ina...Yes 42:6amitundu adzafika ku kuunika kwako...Yes 60:3chuma cha anthu amitundu ina...Yes 61:6anthu akunja azifunitsa zonsezi...Mat 6:32musapite kwa anthu amitundu ina...Mat 10:5kuwala kodzaunikira anthu a amitundu...Luk 2:32amitundu akwaniritsidwa...Luk 21:24akalalikire dzina langa anthu amitundu...Mac 9:15pa amitundunso panathiridwa mphatso...Mac 10:45kuunika kwa amitundu...Mac 13:47lichitidwa mwano pakati pa anthu amitundu...Aro 2:24ndiyenso Mulungu wa anthu amitundu ina...Aro 3:29sichimveka mwa amitundu...1 Akor 5:1chinsinsi pakati pa amitundu...Akol 1:27mphunzitsi wa amitundu...1Timoteo 2:7osalandira kanthu kwa amitundu...3 Yoh 7[onaninso: akunja]

AMITUNDU (nations)pakati pa amitundu...Num 23:9aphokoserenji amitundu...Mas 2:1ndidzakupatsa amitundu akhale...Mas 2:8amitundu onse adzamtumikira...Mas 72:11amitundu onse adzamutcha...Mas 72:17amitundu adzaopa dzina la...Mas 102:15pamwamba pa amitundu onse...Mas 113:4amitundu onse ali chabe...Yes 40:17ndani mfumu ya amitundu...Yer 10:7amitundu ambiri adzaphatikidwa...Zek 2:11phunzitsani anthu amitundu...Mat 28:19akuchiritsa nao amitundu...Chiv 22:2

AMOWABU (Moabites)zidzukulu za Loti...Gen 19:36,37anakhalira limodzi ndi Midiyani potemberera Israeli...Num22:4anachotsedwa kuchokera mu Israeli...Deut 23:3-6

anachitira chifundo Rute...Rut 1:4anagonjetsedwa ndi Israeli...1Sam 14:47;2 Sam 8:2;2Maf 3:4-27azimai ake, anamusokeletsa Solomoni...1 Maf 11:1-8uneneri wokhudza Amowabu...Yes 11:14;15:1-9;Yer48:1-47;Amosi 2:1-3

AMOYO (living)m’kuunika kwa amoyo...Mas 56:13amoyo adziwa kuti tidzafa...Mlal 9:5akhale woweruza amoyo...Mac 10:42amene adzaweruza amoyo...2 Tim 4:1mau a Mulungu ali amoyo...Aheb 4:12[onaninso: wamoyo]

AMUNA (husbands)akafunse amuna ao...1 Akor 14:35amuna, muzikonda akazi...Aef 5:25

AMUNA (men)amuna okha okha anachitirana...Aro 1:27[onaninso: anthu]

ANA A NG’OMBE (calves)napanga ana ang’ombe awiri...1 Maf 12:28kutumphatumpha ngati ana ang’ombe...Mal 4:2wa mbuzi ndi ana ang’ombe...Aheb 9:12mwazi wa ana ang’ombe...Aheb 9:19

ANA ACHISAMBA (first born)chauta adapha ana onse achisamba...Eks 12:29[onaninso: mwana wachisamba, wobadwa woyamba]

ANA AKAZI (daughters)ndipo anabala ana amuna ndi akazi...Gen 5:4anayang’ana ana akazi...Gen 6:2ana anu amuna ndi akazi adzanenera...Mac 2:17munthuyu anali nao ana akazi anai...Mac 21:9mudzakhala kwa ine ana amuna ndi akazi...2 Akor 6:18

ANA (babes)ndipo ndidzapereka ana...Yes 3:4

ANA (brood)ana a njoka inu...Mat 12:34monga nkhuku imasonkhanitsa anapiye...Luk 13:34

ANA (children)sakubalira ana Yakobo...Gen 30:1nonsenu ndinu ana a Mulungu...Mas 82:6ana ndi mpahatso yochokera kwa Chauta...Mas 127:3anadalitsa ana anu...Mas 147:13Ana a Ziyoni asekere...Mas 149:2anake adala pambuyo pake...Miy 20:7anake adzanyamuka...Miy 31:28akukuponderezani ndi ana chabe...Yes 3:12ana amene Chauta wandipatsa...Yes 8:18ana ako ndidzawadalitsa...Yes 54:13ana anga amene sadzandinyenga...Yes 63:8adzayanjanitsa ana ndi atate...Mal 4:6ana adzaukira makolo awo...Mat 10:21kusintha ndi kusanduka ngati ana...Mat 18:3ankabwera ndi ana kuti Yesu...Mat 19:13alekeni anawa adzibwera kwa ine...Mat 19:14adawapatsa mpamvu zoti akhale ana...Yoh 1:12mukadakhala ana a Abrahamu...Yoh 8:39kutsimikiza kuti ndife ana a Mulungu...Aro 8:16ndinu ana anga okondedwa...1Akor 4:14khalani ngati ana osadziwa...1Akor 14:20pakuti si udindo wa ana...2 Akor 12:14sitidzakhalanso ngati ana...Aef 4:14yendani monga ana a kuunika...Aef 5:8

Page 13: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ana a Mulungu opanda chilema...Afil 2:15ndife ana a Mulungu tsopano...1Yoh 3:2kuti timakonda ana a Mulungu...1Yoh 5:2koposa kumva kuti ana akuyenda...3 Yoh 4

ANA (offspring)amuberekere ana...Mat 22:24ofumira mwa iye ngati ana...Mac 17:28[onaninso: zidzukulu]

ANA (sons)ana ake akamalemekezedwa...Yob 14:21ana ako amuna...Yes 60:4alibe ana amuna...Yer 49:1“ana a Mulungu wamoyo,”...Hos 1:10mudzakhala ana a Mulungu...Luk 6:35chikukhudza inu ana ake...Mac 3:25amenewo ndi ana ake...Aro 8:14omwe ali ana enieni...Agal 3:7kuti potero asanduke ana...Agal 4:5kutsimikiza kuti ndinu ana...Agal 4:6adafuna kufikitsa ana...Aheb 2:10amakulankhulani ngati ana...Aheb 12:5amachitira ndi ana ake...Aheb 12:8

ANAMWALI (maidens)anyamata pamodzi ndi anamwali...Mas 148:12

ANENERI (prophets)Chauta akadakhala aneneri...Num 11:29Saulonso ali m’gulu la aneneri...1 Sam 10:12kudzera mwa aneneri ake onse...1 Maf 22:22ali kuti aneneri anu...Yer 37:19ulose zodzudzula aneneri...Ezek 13:2aneneri ake anali achabechabe...Zef 3:4ndiponso zophunzitsa za aneneri...Mat 5:17a Mose ndiponso aneneri...Mat 7:12kapena m’modzi mwa aneneri...Mat 16:14mumakonza bwino manda a aneneri...Mat 23:29ine ndidakutumizirani aneneri...Mat 23:34Yerusalemu umapha aneneri...Mat 23:37kudzaoneka aneneri onama...Mat 24:11mabuku a Mose ndi aneneri...Luk 16:29inu ndinu ana a aneneri...Mac 3:25aneneri onse adamchitira umboni...Mac 10:43mumakhulupirira mau a aneneri...Mac 26:27kale kudzera mwa aneneri...Aro 1:2Mulamulo ndi aneneri omwe...Aro 3:21anthu amenewa adapha aneneri...Aro 11:3ena aneneri, ena alaliki...Aef 4:11kumbukirani chitsanzo cha aneneri...Yak 5:10aneneri amene adaneneratu...1 Pet 1:10panali aneneri ena onama...2 Pet 2:1aneneri ambiri onama awanda...1Yoh 4:1a Mulungu ndi a aneneri...Chiv 16:6mudapezeka magazi a aneneri...Chiv 18:24ngati abale ako aneneri...Chiv 22:9

ANIKOLAI (Nicolaitans)gulu lophunzitsa makhalidwe oipa...Chiv 2:6-15

ANKHONDO (armies)ndinyoza makamu ankhondo...1 Sam 17:10magulu ake ankhondo...Yob 25:3kuperekeza ankhondo athu...Mas 60:10mwakuti idatuma ankhondo ake...Mat 22:7magulu ankhondo...Luk 21:20ndipo magulu ankhondo...Chiv 19:14ndi magulu ankhondo ao...Chiv 19:19

ANKHONDO (army)chiwerengero cha ankhondo...Chiv 9:16

[onaninso: gulu la ankhondo]

ANSEMBE (priests)onditumikira ine ngati ansembe...Eks 19:6ansembe saphunzitsa opanda...Mika 3:11ngati mtundu wa ansembe...Chiv 1:6adzakhala ansembe a Mulungu...Chiv 20:6

ANSEMBE (priesthood)kuti mukhale ansembe oyera mtima...1 Pet 2:5ansembe achifumu...1 Pet 2:9[onaninso: unsembe]

ANTHU AKUNJA (heathen)amachitira anthu akunja...Mat 6:7umuyese munthu wakunja...Mat 18:17

ANTHU AM’NDENDE (prisoners)kubuula kwa anthu am’ndende...Mas 79:11ndine womangidwa m’ndende...Aef 3:1amene ndili m’ndende...2 Tim 1:8am’ndende akupeza nawo...Yob 3:18Chauta amamasula am’ndende...Mas 146:7muzikumbukira am’ndende...Aheb 13:3

ANTHU AMALONDA (merchants)mu mzinda wa anthu amalonda...Ezek 17:4mudachulukitsa anthu anu amalonda...Nah 3:16amalonda anali anthu otchuka...Chiv 18:23

ANTHU (flesh)anakumbukira kuti iwo ndiwo anthu...Mas 78:39ndipo anthu onse adzaona...Yes 40:5anthu onse ndi udzu...Yes 40:6Mzimu wanga pa anthu onse...Yow 2:28ndipo anthu onse adzaona...Luk 3:6[onaninso: mnofu, thupi]

ANTHU (men)anthu anayamba kutchula dzina...Gen 4:26anayang’ana ana akazi a anthu...Gen 6:2mudzafa monga anthu...Mas 82:7Aigupto ndiwo anthu...Yes 31:3ndidzakusandutsani asodzi a anthu ...Mat 4:19mtendere pansi pano mwa anthu...Luk 2:14kodi, kapena kwa anthu...Luk 20:4m’modzi adzitamande mwa anthu...1 Akor 3:21kutumikira Yesu Khristu, si anthu...Aef 6:7pakati pa Mulungu ndi anthu...1Timoteo 2:5[onaninso: amuna]

ANTHU (people)inu mudzakhala anthu anga...Eks 6:7anthu akwanu ndiwo anthu...Rut 1:16odala anthu odziwa...Mas 89:15ndife anthu ake ndi nkhosa...Mas 100:3odala anthu akuona zotere...Mas 144:15odalitsika Aigupto anthu anga...Yes 19:25ali anthu opanduka...Yes 30:9anthu amene andiputa ine...Yes 65:3nadzakhala anthu anga...Yer 24:7inu sindinu anthu anga...Hos 1:9kudzakhala monga anthu...Hos 4:9kukonzeratu Ambuye anthu...Luk 1:17atenge mwa iwo anthu...Mac 15:14amene sanakhala anthu anga...Aro 9:25ndi iwo adzakhala anthu anga...2 Akor 6:16anthu akhale ake enieni...Tit 2:14Ambuye adzaweruza anthu...Aheb 10:30koma tsopano muli anthu a Mulungu...1 Pet 2:10anthu a mafuko onse...Chiv 5:9cha Mulungu chiri mwa anthu...Chiv 21:3

Page 14: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ANTIOKEYA (Antioch)— Ku Siriya:kumene mpingo woyamba wa amitunduunakhazikitsidwa...Mac 11:19-21ophunzira anatchedwa kwa nthawi yoyamba kutiAkhristu...Mac 11:26Mpingo utuma Paulo...Mac 13:1-4;15:35-41mzinda womwe mpingo unazunguzidwa ndi anthu a kuYudeya...Mac 15:1-4, Agal 2:11-12— Ku Pisidiya:Paulo anapitako, Ayuda anakana uthenga wabwino...Mac13:14,42-51

ANYAMATA (boys)mudzadzaza ndi ana, anyamata...Zek 8:5

ANZAO (companions)akuru ako apanduka, ali anzao...Yes 1:23amene ali kuitana anzao...Mat 11:16chikondwerero chenicheni koposa anzanu...Aheb 1:9

APAWIRIPAWIRI (double minded)ndimadana nawo anthu apawiripawiri...Mas 119:113iyeyo ndi wa mitima iwiri...Yak 1:8inu anthu okayikakayika...Yak 4:8

APERIZI (Perizzites)umodzi wa mitundu isanu ndi iwiri ya ku Kanani...Deut 7:1anatenga Palestina nthawi ya Abrahamu...Gen 13:7Yakobo anawaopa...Gen 34:30ambiri a iwo anaphedwa ndi Yuda...Ower 1:4,5

APHUNGU (counselors)pochuluka aphungu...Miy 11:14

APHUNZITSI A MALAMULO (scribes)ankachitira aphunzitsi a malamulo...Mat 7:29aphunzitsi a malamulo ndi afarisi...Mat 23:13nawoni aphunzitsi a malamulo...Marko 12:38

APHUNZITSI (teachers)kumvetsa kupambana aphunzitsi...Mas 119:99aneneri, kachitatu aphunzitsi...1 Akor 12:28ena abusa ndi aphunzitsi...Aef 4:11anafuna kukhala aphunzitsi...1 Tim 1:7ofuna kukhala aphunzitsi...Yak 3:1padzoneka aphunzitsi onama...2 Pet 2:1

APOLIYONI (Apollyon)mngelo wa kuphompho...Chiv 9:11

APOLO (Apollos)myuda wa ku Alesandreya, anatumizidwa ku Akaya...Mac18:24-28akunenedwa kukhala ngati anatumikira ku Akorinto...1 Akor1:12;3: 4,22;4:6;16;12

APULUMUTSI (deliverers)apulumutsi akuwapulumutsa...Neh 9:27

ARABU (Arabia)umapereka msonkho kwa Solomoni...1 Maf 10:14,15analanda Yerusalemu...2 Mbir 21:16,17unagonjetsedwa ndi Uziya...2 Mbir 26:1,7unakanidwa ndi Aneneri...Yes 21: 13-17

ARARATI (Ararat)malo amene chombo cha Nowa chinafikira...Gen 8:4achiwembu anathawirako...2 Maf 19:37,Yes 37:38

ARAUNA (Araunah/Ornan)

Muyebusi...2 Sam 24:15-25malo ake opunthirapo tirigu anagulidwa ndi Davide...2Sam 24:18-25malo ake panamangidwa kachisi...2 Mbir 3:1amatchedwanso kuti Oronani...1 Mbir 21:18-28

AREOPAGI (Areopagus)kumene Paulo analalika...Mac 17:18-34

ARI (Ar)mzinda waukulu wa Amoabu...Num 21:15unali mnjira yopita ku Israeli...Deut 2:18unaonongedwa ndi Sihoni Num 21:28unaonongedwa ndi Mulungu...Yes 15:1

ARIKELAO (Archelaus)mwana wamwamuna wa Herodi wamkuru...Mat 2:22

ARINONI (Arnon)malire pakati pa Moabu ndi Aamori...Num 21:13,26malire a Rubeni...Deut 3:12,16Aamori anakumbutsidwa za malo amenewa...Ower 11:18-26

ARIPAKASADI (Arphaxad)mwana wa mwamuna wa Semu...Gen 10:22,24anabadwa zaka ziwiri patatha chigumula...Gen 11:10-13ali mumndandanda wa makolo aYesu...Luk 3:36

ARISTARKO (Aristarchus)Khristu wa ku Makedoniya...Mac 19:29anayenda limodzi ndi Paulo...Mac 20:1,4anamangidwa limodzi ndi Paulo...Akol 4:10

ARITASASTA (Artaxerxes)Aritasasta woyamba, mfumu ya Peresiya (465-425 B.C)analamulira Ezara kupita ku Yerusalemu Ezara 7:1-28kwanthawi yochepa, anaipidwa ndi nkhani ya kumangidwansokwaYerusalemu...Ezara 4: 7-23Analola ulendo wa Nehemiya...Neh 2:1-10analola Nehemiya kubwerera... Neh 13:6

AROERI (Aroer)mzinda kummwera kwaYordane, unamangwidwanso ndi aGadi...Num 32:34, Deut 2:36wopatsidwa kwa Arubeni...Deut 3:12,16wolamuliridwa ndi a Amori...Yos 2:12;13:9,10,16

ARTEMI (Artemis)wopembedzedwa wa ku Efeso, anayambitsa mapokoso...Mac19:23-41

ASA (Asa)mfumu yachitatu ya Yuda, anabwezeretsa kupembedzakoonadi...1 Maf 15:8-15;2 Mbir 14-15Anatuma Benihadadi kulimbana ndi Basa; anadzudzulidwandi mneneri...1 Maf 15:16-22;2 Mbir 16:1-10anali ndi matenda, anapita kwa msing’anga m’malo mwaYehova...2 Mbir 16:12imfa ndi kuikidwa kwake...2 Mbir16:13,14

ASADUKI (Sadducces)anakanidwa ndi Yohane...Mat 3:7anamuyesa Yesu...Mat 16:1-12anakhazikidwa chete ndi Yesu...Mat 22:23-34anasokonezedwa ndi chiphunzitso cha chiukitso...Mac 4:1,2anawatsutsa atumiki...Mac 5:17-40

ASAFU (Asaph)mtsogoleri wa gulu loyimba ...1Mbir 15:16-19;16:1-7;2 Mbir5:6,12anauzidwa kuti ayimbire Yehova Masalimo khumi ndiawiri...2 Mbir 29:30,Mas 50:73-78

Page 15: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ASAHELI (Asahel)mdzukulu wa Davide, mkulu wa nkhondo, anali wa nzeru...2Sam 2:18;23:24,1 Mbir 2:16;27:7anaphedwa ndi Abineri...2 Sam 2:19-23Yoabu anabwezera kuphedwa kwake...2 Sam 3:27,30

ASANU (five)asanu anali opusa...Mat 25:2[onaninso: isanu, zisanu]

ASANU NDI ATATU (eight)owerengeka okha, asanu ndi atatu...1 Pet 3:20

ASENATI (Asenath)mwana wamkazi wa Potifera, mkazi wa Yosefe...Gen 41:45make a Manase ndi Efraimu...Gen 41:50-52;46:20

ASERI (Asher)mwana wamwamuna wa Yakobo kudzera mwa Zilipa...Gen20:12,13anapita ku Egipito ndi Yakobo...Gen 46:8,17anadalitsidwa ndi Yakobo...Gen 49:20— Fuko la:limodzi la mafuko khumi ndi awiri a Israelipanali kalembera wa a Aseri...Num 1:41;26:47anachedwa kumenyana ndi a Kanani...Ower 1:31-32;5:17anali pakati pa ankhondo a Gideoni...Ower 6:35;7:23anali pakati pa anthu a Mulungu ochepa amene anatsala...2Mbir 30: 11

ASIDODI (Ashdod)umodzi wa mizinda isanu ya a Filisti...Yos 13:3mpando wa Dagoni (fano)...1 Sam 5:1-8anatsutsana ndi Nehemiya...Neh 4:7azimayi ochokera mumzinda umenewu ankakwatirana ndiAyuda...Neh 13:23,24wotchedwanso Azotu...Mac 8:40

ASIKELONI (Ashkelon)umodzi wa mizinda isanu ya a Filisti...Yos 13:3, Yer 47:5,7unagonjetsedwa ndi kugwidwa ndi Yuda...Ower 1:18anthu amuzinda umenewu anaphedwa ndi Samsoni...Ower14:19,20unatengedwanso ndi Afilisti...1 Sam 6:17;2 Sam 1:20kuonongedwa kwake kunaneneredwa ndi aneneri...Yer 47:5,7,Amosi 1:8, Zef 2:4,7, Zek 9:5

ASILIKALI (soldiers)asilikali adayamba kumseka...Luk 23:36asilikali adaluka msangamutu...Yoh 19:2

ASING’ANGA (physicians)muli ngati asing’anga...Yob 13:4chonse kulipira asing’anga...Luk 8:43

ASITAROTI (Ashtaroth)mzinda mu Basani womwe mfumu Ogi imakhala...Deut1:4,Yosw 12:4unagwidwa ndi Israeli...Yos 9:10— komwe akazi a ku Kanani amatengera miyambo yawo...1Sam 7:3,4; 31:10

ASITAROTE (Ashtoreth)mulungu wamkazi wa Afilsti...1 Sam 31:10chimapembedzedwa ndi Solomoni...1 Maf 11:5,33chinaonongedwa ndi Josiya...2 Maf 23:13

ASIYA (Asia)Paulo analetsedwa kuti alalikireko...Mac 16:6kumene Paulo analalikirako pamapeto pake...Mac 19:1-26

kumene kunali mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 1:4,11

ASODZI A NSOMBA (fishermen)asodzi adzadandaula ndi kulira...Yes 19:8okhala ngati asodzi a nsomba...Yer 16:16ndikakusandutsani asodzi...Mat 4:19

ASURI (Asshur/Assyria)mmodzi wa ana amuna a Semu...Gen 10:22ali mndandanda wa makolo a Asuri...1 Mbir 1:17— mulungu wamkulu wa Asuri, owoneka m’maina mongaOsinipara...Ezara 4:10— mzinda mu Asiriya kapena dziko la Asuri...Num 24:22,24lidayambika ndi Nimrode...Gen 10:8-12,Mik 5:6mtumiki wa zolinga za Mulungu...Yes 7:17-20anagonjetsa a Israeli...2 Maf 15:19,20,29;17:3-41anawopseza Yuda...2 Maf 18:13-37Hezekiya anapemphera kwa Mulungu, ankhondo anaphedwamozizwitsa...2 Maf 19: 1-35ananeneredwa...Num 24:22-24,Yes10:12-19,14:24,25,19:23-25;Hos 10:6;11:5,Nah 3:1-19

ATALIYA (Athaliah)mwana wamkazi wa Ahabu ndi Yezebele...2 Maf 8:18,26;2Mbir 22:2,3anapha ana achifumu, nalanda mpando...2 Maf 11:1-3;2 Mbir22:10,11anaphedwa pakuyambika kwa nsembe ...2 Maf 11: 4-16;2Mbir 23:1-21

ATATE (fathers)simukhala ndi atate ambiri...1 Akor 4:15[onaninso: makolo]

ATATE (father’s)mu ufumu wa Atate wanga...Mat 26:29ndikhale m’zache za Atate wanga...Luk 2:49mnyumba mwa Atate anga...Yoh 14:2wina ali naye mkazi wa atate ache...1 Akor 5:1

ATENE (Athens)Paulo analalikirako...Mac 17:15-34Paulo anakhalako...1 Ates 3:1

ATSOGOLERI (guides)atsogoleri akhungu...Mat 23:16

ATUMIKI (deacons)pamodzi ndi oyang’anira ndi atumiki...Afil 1:1atumiki akhale olemekezeka...1 Tim 3:8atumiki akhale mwamuna wamkazi m’modzi...1 Tim 3:12

ATUMIKI (ministers)amoto mumawasandutsa atumiki...Mas 104:4iwo ndiwo atumiki a Mulungu...Aro 13:6ife tokha monga atumiki a Mulungu...2 Akor 6:4kodi ali atumiki a Khristu...2 Akor 11:23

ATUMIKI (servants)sakhulupirira ndi atumiki...Yob 4:18ndinu atumiki a Mulungu...Yes 61:6[onaninso: akapolo]

ATUMWI (apostles)maina awo a atumwi...Mat 10:2anawatchanso dzina lao atumwi... Luk 6:13anaoneketsa ife atumwi...1 Akor 4:9wamng’ono wa atumwi...1Akor 15:9sindinaperewera konse ndi atumwi...2 Akor 11:5otere ali atumwi onyenga...2 Akor 11:13koma wina wa atumwi...Agal 1:19

Page 16: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

adzitcha okha atumwi...Chiv 2:2ndi atumwi...Chiv 18:20

AULAMULIRO (principality)mafumu onse, aulamuliro onse...Aef 1:21wolamulira maulamuliro...Akol 2:10

AUMPHAWI WAUMPHAWI (needy)ozunzika anu ndi aumphawi...Deut 15:11apambukitsa aumphawi mnjira...Yob 24:4nthawi zonse waumphawi...Mas 9:18adzapulumutsa waumphawi...Mas 72:12nakweza waumphawi kumchotsa...Mas 113:7anthu anga aumphawi...Yes 10:2aumphawi nadzagona pansi...Yes 14:30mwakhala linga la aumphawi...Yes 25:4

AVENE (Aven)mzinda wa Oni mu Aigupto kufupi ndi Kairo...Gen41:45;Ezek 30:17— dzina loyerekezedwa Beteli...Hos 10:5,8— chigwa mu Asuri...Amo 1:5

AZARIYA (Azariah)mneneri amene analimbikitsa mfumu Asa...2 Mbir 15:1-8— mwana wamwamuna wa mfumu Yehosofati...2 Mbir 21:2— mfumu ya Yuda...2 Maf 15:1— mkulu wansembe yemwe anadzudzula Uziya...2 Mbir 26:16-20— wamkulu wansembe nthawi ya Hezekiya...2 Mbir 31:9,10— Dzina la chihebri la Abidinego...Dan 1:7

AZEKA (Azekah)malo omwe Goliati ndi ankhondo a Afilisti anamangazithando zawo...1 Sam 17:1,4,17mzinda wolandidwa ndi Nebukadinezara...Yer 34:7

AZEZE (harps)akuimba azeze...Chiv 14:2tinapachika mazeze athu...Mas 137:2

AZIMAVETI (Azimaveth)Mudzi pafupi ndi Yerusalemu...Neh 12:29Wotchedwanso Bete-Azimaveti...Neh 7:28

BBAALA PERAZIMU (Baal Perazim)

malo omwe Davide anagonjetsa Afilisti...2 Sam 5:18-20chimodzimodzinso ndi Perazimu...Yes 28:21

BAALA ZEBUBU (Baal zebub)mulungu wa Afilisti ku Ekroni...2 Maf 1:2amene Ahaziya anafunsira...2 Maf 1:2,6,16wotchedwanso Beelzebule...Mat 10:25;12:24

BAALA PEORI (Baal Peor)mulungu wa Amoabu; anapembedzedwa ndi a Israeli...Num25:1-9

BAALA (Baalah)mzinda wotchedwanso Kiriyati-Yearimu...Yos 15:9,10

BAALA (Baal)mulungu wamwamuna wa a Fonika ndi a Kanani...2 Mafumu23:5anali ndi mapembedzedwe ake...1Maf 18:26,28;19:18;Mas106:28;Yer 7:9;19:5;Hos 9:10;13:1,2Aisraeli anampembedza...Num 25:1-5;Ower2:11-14;3:7;6:28-32;1Maf 16:31,32;2 Maf 21:3;Yer 11:13; Hos 2:8

Ahazi anapanga mafano ake...2 Mbir 28:1-4anachotsedwa ndi Eliya...1Maf 18:17-40anachotsedwa ndi Yosiya...2 Maf 23:4,5anachotsedwa ndi aneneri...Yer 19:4-6;Ezek 16:1,2,20,21mbiri ya zinthu za m’mbuyo zokumbukiridwa...Aro 11:4

BAANA (Baanah)amene anapha Isiboseti...2 Sam 4:1-12

BABELE, NSAJA YA (Babel, tower of)nsanja yomangidwa kuti chikweze munthu ndi kusungaumodzi wa mitundu...Gen 11:1-4zolinga zao zinalepheretsedwa ndi Mulungu...Gen 11:5-9

BABULO (Babylon)womangidwa ndi Nimrode; nsaja ya Babele...Gen10:8-10;11:1-9wanenedwa pa...Yes 13:19;14:4;Yer 51: 44;Dan 4:30kumene Ayuda anatengedwera ukapolo...2 Maf 25:1-21;2Mbir 36:5-21anthu okhalamo, anafotokozedwa...Yes 47:1,9,13;Yer50:35-38;Dan 5:1-3ananeneredwa...Yes 13:1-22;Yer 21:1-7;25:9-12;27:5-8;Yer50:1-46;Dan 2:31-38;7:2-4mzinda wa uneneri...Chiv 14:8;16:9;17:1-18

BADWA (birth)liposa tsiku lakubadwa...Mlal 7:1ndipo kubadwa kwake kwa...Mat 1:18adzakondwera pakubadwa kwake...Luk 1:14anaona munthu ali osaona chibadwire...Yoh 9:1

BADWA (born)ana amuna onse akabadwa...Eks 1:22koma munthu abadwira mavuto...Yob 5:7munthu wobadwa ndi mkazi...Yob 14:1uyu anabadwa komweko...Mas 87:4mphindi yakubadwa...Mlal 3:2mwana wakhanda wabadwa...Yes 9:6kodi dziko lidzabadwa...Yes 66:8anabadwa mwa iye...Mat 1:16pakuti wakubadwirani inu...Luk 2:11munthu sabadwa mwatsopano...Yoh 3:3chobadwa m’thupi...Yoh 3:6ndinabadwira ichi ine...Yoh 18:37anabadwa monga mwa thupi...Agal 4:23amene munabadwanso...1 Pet 1:23abadwa kuchokera kwa Mulungu...1 Yoh 4:7wabadwa kuchokera kwa Mulungu...1 Yoh 5:1wabadwa kuchokera kwa Mulungu...1 Yoh 5:18

BADWA (conceived)ndinabadwa m’mphulupulu...Mas 51:5[onaninso: ima, pathupi]

BALA (bear)amene Sara adzabalira iwe...Gen 17:21nadzabala mwana wamwamuna...Mat 1:23mkazi wako adzakubalira mwana...Luk 1:13nthambi iliyonse ya mwa ine yosabala...Yoh 15:2[onaninso: nyamula]

BALA (begets)wobala chitsiru adzachititsa manyazi...Miy 17:21wobala mwana wanzeru...Miy 23:24chinkana munthu akabala...Mlal 6:3

BALA (begotten)ine lero ndakubala...Mas 2:7ndani wandibalitsa ine amenewa...Yes 49:21monga ndinabala inu mwa uthenga wabwino...1 Akor 4:15anatibalanso kuchiyembekezo cha moyo...1 Pet 1:3

Page 17: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

iye amene anabala akondanso iye amene...1 Yoh 5:1

BALA (birth)anachibala ndani...?...Yob 38:29mpaka nthawi yobala...Yes 66:9ibala nisiya ana ake...Yer 14:5pamenepo chilakolako chitaima chibala uchimo...Yak 1:15

BALA (bore)anatenga pakati, nabala Kaini...Gen 4:1ndi kwa Sara amene anakubalani...Yes 51:2ndipo anabala mwana...Chiv 12:5[onaninso: bereka, nyamula, senza]

BALAKI (Balak)mfumu ya Amoabu...Num 22:4anatuma Balamu kuti akatemberere Israeli...Num 22:24

BALALIKA (Dispersion)kwa Ahelene obalalikawo...Yoh 7:35alendo a chibalaliko...1 Pet 1:1

BALALITSA (scatter)ndidzakubalalitsani pakati...Lev 26:33abalalitseni anthu okonda...Mas 68:30ndidzawabalalitsa kumphepo...Yer 49:32mwabalalitsa ndi kumwaza...Yer 23:2amene anawabalalitsa...Yer 31:10pamene mudzabalalikana...Yoh 16:32[onaninso: mwaza]

BALAMU (Balaam)anatumizidwa ndi Balaki kuti akatemberere Israeli...Num22:5-7;Yosw24:9analepheretsedwa ndi bulu yemwe analankhula...Num22:22-35;2 Pet 2:16temberero linasanduka dalitso...Deut 23:4,5;Yosw24:10ananeneredwa...Num 23:7-10,18-24;24:3-9,15-24amafaniziridwanso ku chipangano chatsopano...2 Pet2:15,16;Yuda11;Chiv 2:14

BAMBO (father)ndi mkazi wa bambo wake...1 Akor 5:1

BANGA (spot)wopanda banga...Aef 5:27[onaninso: chilema]

BANGO (flax)bango lopindika sadzalithyola...Yes 42:3sadzatsiriza bango lothyoka...Mat 12:20

BANGULA (roar)misona ya mikango imabangula...Mas 104:21ndidzawabangulira mkango...Hos 11:10kodi mkango umabangula...Amo 3:4ngati kubangula kwa mkango..Miy 19:12umakhalira mkango wobangula...Miy 28:15ngati mkango wobangula...1 Pe 5:8[onaninso: kokoma]

BANJA (house)kapena banja logawanika...Mat 12:25[onaninso: nyumba]

BANJA (household)mayendedwe a banja lake...Miy 31:27ndipo a pa banja ake a munthu...Mat 10:36anabatizidwa iye ndi a pa banja...Mac 16:15udzapulumuka iwe ndi a pa banja ako...Mac 16:31koma ndinabatizanso a pa banja...1 Akor 1:16makamaka iwo a pa banja la...Agal 6:10

makamaka iwo a pa banja la Kaisara...Afil 4:22[onaninso: nyumba]

BAR-YONA (Bar-Jonah)dzina la bambo ake a Simoni (Petro)...Mat 16:17

BAR YESU (Bar-Jesus)mneneri wonyenga wa Chiyuda...Mac 13:6-12

BARABA (Barabbas)wakupha yemwe anamasulidwa m’malo mwa Yesu...Mat27:16-26;Mac 3:14,15

BARAKI (Barak)anagonjetsa Yabini...Ower 4:1-24munthu wa chikhulupiriro...Aheb 11:32

BARATIMEO (Bartimaeus)wakhungu wopemphapempha yemwe anachiritsidwa ndiYesu...Marko 10:46-52

BARELE (Barley)dziko la tirigu ndi barele...Deut 8:8mtanda wa mkate wa barele...Ower 7:13pakuyamba anthu kucheka barele...Rut 1:22amene ali nayo mikate isanu ya barele...Yoh 6:9ndi miyeso itatu ya barele yogula rupiya ndi mafuta ndi

vinyo...Chiv 6:6

BARIZILAI (Barzillai)anam’bweretsera Davide chakudya...2 Sam 17:27-29chifukwa chakukalamba analephera kumtsatira Davide...2Sam 19:31-39

BARNABA (Barnabas)wophunzira wochokera ku Kupro, anapereka zinthuzake...Mac 4:36,37anamthandizira Paulo...Mac 9:27anatumikira ku Antiokeya...Mac 11:22-30anayenda ndi Paulo...Mac 12:25;13-15analekana ndi Paulo chifukwa cha Yohane Marko...Mac15:36-39

BARSABASI (Barsabas)anasankhidwa kupikisana pa chisankho chosankha mlowam’malo mwa Yudasi...Mac 1:23anatumizidwa ku Antiokeya...Mac 15:22

BARTOMEO (Bartholomew)wotchedwa Natanaele...Yoh 1:45,46m’modzi wa ophunzira khumi ndi awiri a Yesu...Mat 10:3;Mac 1:13

BARUKI (Baruch)mwana ma mwamuna wa Neriya...Yer 32:12,13mnzake wa Yeremiya wokhulupirika...Yer 36:4-32

BASA (Baasha)analanda ufumu wa Israeli; analamulira moipa, anamenyanandi Yuda...1 Maf 15:16-16:7

BASANI (Bashan)anagonjetsedwa ndi Israeli...Num 21:33-35anapatsidwa kwa Manase...Deut 3:13anagonjetsedwa ndi Hazaele, mfumu ya Siriya...2 Maf10:32,33

BATA (calm)nyanja idzachitira inu bata...Yon 1:12ndipo panagwa bata lalikuru...Mat 8:26

BATA (still)

Page 18: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mumachititsa bata...Mas 65:7a panyanja adachita bata...Mas 107:29“tonthola, khala bata...Marko 4:39[onaninso: chete]

BATESEBA (Bathsheba)mkazi wa Uriya, anatengedwa ndi Davide...2 Sam 11mwana wake woyamba anamwalira...2 Sam 12:14-19Anabala Solomoni...2 Sam 12:24anateteza mpando wa ufumu wa Solomoni...1 Maf 1:15-31ananyengezedwa ndi Adoniya...1 Maf 2:13-25

BATIZA (baptize)inetu ndinakubatizani inu...Mat 3:11koma ubatiza bwanji...Yoh 1:25angakhale Yesu sanabatiza...Yoh 4:2sindinatuma ine kubatiza...1 Akor 1:17[onaninso: ubatizo,batizidwa, maubatizo]

BATIZIDWA (baptized)ndiyenera ine kubatizidwa ndi inu...Mat 3:14amene akhulupirira nabatizidwa...Marko 16:l6nawabatiza koposa Yohane...Yoh 4:1lapani, batizidwani...Mac 2:38nabatizidwa pomwepo...Mac 16:33anamva nakhulupirira, nabatizidwa...Mac 18:8nubatizidwe ndi kusamba...Mac 22:16tonse amene tinabatizidwa...Aro 6:3sindinabatiza m’modzi yense...1 Akor 1:14koma ndinabatizanso a banja langa...1 Akor 1:16nabatizidwa onse kwa Mose...1 Akor 10:2ife tonse tinabatizidwa...1 Akor 12:13iwo amene anabatizidwa...1 Akor 15:29pakuti nonse amene munabatizidwa...Agal 3:27[onaninso: ubatizo,batiza, maubatizo]

BAYA (pierce)chidzabaya mtima wanu...Luk 2:35

BEELZEBULE (beelzebub)Yesu ananenedwa kuti amamtumikira...Mat 10:25;12:24-27

BEERELAHAYI-ROYI (Beer-Lahai-Roi)malo amene mngelo anakomana ndi Hagara...Gen 16:7-14komwe Isake amakhala...Gen 24:62

BEERESEBA (Beersheba)malo amene Mulungu anaonekera kwa Hagara...Gen 21:14-19Mulungu anaonekera kwa Isake...Gen 26:23-25Mulungu anaonekera kwa Yakobo...Gen 46:1-5Mulungu anaonekera kwa Eliya...1 Maf 19:3-7malumbiro analumbiridwa pamenepo ndi Abrahamu...Gen21:31-33malumbiro analumbiridwa ndi Isake...Gen 26:26-33

BELI (bel)mulungu wa ku Babulo...Yes 46:1;Yer 50:2;51:44

BELISAZARA (Belshazzar)mfumu ya ku Babulo; Daniele anamasulira maloto ake...Dan 5

BELITSAZARA (Belteshazzar)dzina lachiBabulo la Daniele...Dan 1:7

BENAMMI (Ben-Ammi)mwana wamwamuna wa Loti, tate wa a Ammoni...Gen 19:38

BENAYA (Benaiah)mwana mwamwamuna wa Yehoda, munthu wamphamvu...2Sam 23:20-23wokhulupirika kwa Davide...2 Sam 15:18;20:23anamperekeza Solomoni pokadzodzedwa ufumu...1 Maf

1:38-40ananyonga Adoniya, Yoabu, Simei...1 Maf2:25,29-34,45,46— Benaya mpiratoni; m’modzi wa amuna amphamvu aDavide...2 Sam 23:30kazembe woyang’anira gulu la nkhondo...1 Mbir 27:14

BENIHADADI (Ben-Hadad)mfumu ya ku Damasiko:-woyamba: anatengedwa ndi Asa kuti akagonjetse Basa, mfumu yaIsraeli...1 Maf 15:18-21— wachiwiri: anamenya nkhondo ndi Ahabu, mfumu ya Israeli...1 Maf20 anazunguliridwa ndi ankhondo a ku Samaria...2 Maf6:24-33;7:6-20 anaphedwa ndi Hazaeli...2 Maf 8:7-15— wachitatu: anataya zinthu zonse zomwe anatenga kwa a Israeli ndiHazaeli, tate ake...2 Maf 13:3-25

BENJAMINI (Benjamin)mwana wotsiriza wa Yakobo...Gen 35:16-20anatengedwa kupita ku Ejipito malinga ndi lamulo laYosefe...Gen 42-45ananeneredwa za iye ndi Yakobo...Gen 49:27— fuko lake: mabanja ake...Num 26:38-41anapatsidwa malo...Yos 18:11-28fuko la Saulo...1 Sam 9:1,2fuko la Paulo...Afil 3:5anagwidwa chifukwa chofuna kukhululukira tchimo laGibeya...Ower 20:12-48akazi afukoli anapatsidwa kwa anthu otsala...Ower 21:1-23

BENONI (Ben-Oni)dzina lomwe Rakele anapereka kwa Benjamini...Gen 35:16-18

BEREKA (bore)iye anawaombola, nawabereka nawanyamula...Yes 63:9[onaninso: bala, nyamula, senza]

BEREYA (Berea)mzinda wa ku Makedoniya; omwe Paulo anauchezera...Mac17:10-15

BERNIKE (Bernice)mlongo wa Herodi Agripa wachiwiri...Mac 25:13-23anamvera mau oziteteza a Paulo...Mac 26:1-30

BERODAKI-BALADANI (Berodach-Baladan)mfumu ya ku Babulo...2 Maf 20:12-19[onaninso: Merodaki-Baladani]

BESENI (basin)anathira madzi m’beseni...Yoh 13:5

BETANIYA (bethany)mzinda womwe unali paphiri la Azitona...Luk 19:29kwao kwa Lazaro...Yoh 11:1kwao kwa Simoni wakhate...Mat 26:6Yesu anachezerako...Marko 11:1,11,12kumene Yesu anakwera kupita kumwamba...Luk 24:50,51

BETABARA (Bethabara)kutsidya lina kwa Yordano komwe Yohane amabatizira...Yoh1:28

BETEFAGE (Bethphage)mudzi woyandikana ndi Betaniya...Marko 11:1woyandikira phiri la Azitona...Mat 21:1

Page 19: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

BETELEHEMU (Bethlehem)poyamba amatchedwa Efrati...Gen 35:16Rakelo anaikidwa kumeneko...Gen 35:19kwawo kwa Naomi ndi Boazi...Rut 1:1,19;4:9-11kwawo kwa Davide...1 Sam 16:1-18malo omwe ananeneredwa kuti mesiya adzabadwira...Mika5:2Khristu anabadwira kumeneko...Mat 2:1;Luka 2:4-7;Yoh 7:42kumene ana (makanda) anaphedwa ndi Herodi...Mat 2:16-18

BETELI (Bethel)Abramu anakhala moyandikana naye...Gen 12:7,8kumene kunali guwa la nsembe la Abram...Gen 13:3,4malo omwe Yakobo anaona masomphenya amakwererookwera kumwamba...Gen 28:10-19kumene Yakobo anabwererako...Gen 35:1-5Samuele anaweruza kumeneko...1 Sam 7:15,16malo opembedzera ndi operekera nsembe...1 Sam 10:3malo akuru opembedzera mafano...1 Maf 12:28-33maguwa ake anaonongedwa ndi Yosiya...2 Maf 23:4,15-20unaneneredwa ndi aneneri...1 Maf 13:1-10;Amosi 7:10-13;Yer48:13;Hos 10:15

BETESDA (Bethesda)thamanda m’Yerusalemu...Yoh 5:2-4

BETI SEANI (Beth shan or Beth Sean)mzinda ku Isakara...Yos 17:11-16pamene mtenbo wa Saulo unapachikidwa...1 Sam 31:10-13;2Sam 21:12-14

BETI PEORI (Beth Peor)mzinda womwe unali pafupi ndi Pisiga...Deut 3-29Mose anaikidwa mowuyandikira...Deut 34:6unapatsidwa kwa a Rubeni...Yos 13:15,20

BETI-HORONI (Beth Horon)mizinda iwiri ya Ephraimu...Yos 16:3,5inatetezedwa ndi Solomoni...2 Mbir 8:3,5wotchuka ku nkhondo...Yos 10:10-14;1 Sam 13:18

BETISEMESI (Bethshemesh)kumene likasa linabweretsedwa...1 Sam 6:12-19pamene Yoasi anagonjetsa Amaziya...2 Maf 14:11unatengedwa ndi Afilisti...2 Mbir 28:18

BETSAIDA (Bethsaida)mzinda wa kutsidwa kwa nyanja...Marko 6:45kwawo kwa Andreya, Petro ndi Filipo...Yoh 1:44;12:21munthu wakhungu anachiritsidwa kumeneko...Marko 8:22,23anthu zikwi zisanu anadyetsedwa pafupi ndi mzindaumenewu...Luk 9:10-17kusakhulupirira kwake kunakanidwa...Mat 11:21;Luk 10:13

BEULA (Beulah)chizindikiro cha Israeli woona...Yes 62:4,5

BEZALELE (Bezalel)chidzukulu cha Huri...1 Mbir 2:20womanga chihema...Eks 31:1-11;35:30-35

BI (deep)mumdima woti bi...Miy 20:20[onaninso: kulu, kuya, zama]

BILIDADI (Bildad)m’modzi wa amzake a Yobu...Yob 2:11analankhula katatu...Yob 8:1-22;18:1-21;25:1-6

BILIHA (Bilhah)wantchito (mdzakazi) wa Rakele...Gen 29:29

mai wa Dani ndi Nafutali...Gen 30:1-8anachita choipa pogona ndi mwana wakeRubeni...Gen 35:22

BINGU (thunder)bingu lanu linamveka...Mas 77:18ndili wobisika m’bingu...Mas 81:7mkokomo wa bingu...Mas 104:7oopsa ngati bingu...Marko 3:17kwamphamvu kwa bingu...Chiv 14:2adagunda ngati bingu...2 Sam 22:14adagunda ngati bingu...Mas 18:13akamva mabingu akulira...Eks 20:18kwamphamvu kwa bingu...Chiv 19:6

BISA (conceal)ndi wamphamvu yonse sindidzachibisa...Yob 27:11kubisa kanthu ndi ulemerero...Miy 25:2

BISA (concealed)chilungamo chanu sindinachibisa...Mas 40:10chiposa chikondi chobisika...Miy 27:5

BISA (hide)pamaso panu mudzawabisa...Mas 31:20ndipo musadzibisa pa kupempha...Mas 55:1mukabisa nkhope yanu...Mas 104:29Mulungu, amene mudzibisa nokha...Yes 45:15kuti usadzibisire wekha...Yes 58:7tibiseni ife kunkhope ya iye...Chiv 6:16

BISALIKA (secret)si poonekera koma monga mobisalika...Yoh 7:10[onaninso:bisika, chinsinsi, mtseri]

BISALIRA (hiding)inu ndinu mobisalira mwanga...Mas 32:7monga pobisalira mphepo...Yes 32:2

BISIKA (hidden)zolemera zobisika za m’malo...Yes 45:3komweko kunabisika mphamvu...Hab 3:4kapena kanthu kobisika...Mat 10:26yobisikayo, imene Mulungu...1 Akor 2:7amenenso adzaonetsera zobisika...1 Akor 4:5tikaniza zobisika za manyazi...2 Akor 4:2munthu wobisika wamtima...1 Pet 3:4ndidzampatsa mana obisika...Chiv 2:17

BISIKA (secret)mundimasule kwa zolakwa zobisika...Mas 19:12kuponyera wangwiro mobisika...Mas 64:4ndi zoipa zathu zobisika pounikira nkhope yanu...Mas 90:8chakudya chobisika chikoma...Miy 9:17yokhala m’ming’alu ya thanthwe, mobisika motsetsereka...Nyi2:14ndipo iwo adzadetsa pobisika panga...Ezek 7:22kufuna kutha ozunzika mobisika...Hab 3:14ndidzaulula zinthu zobisika chiyambire...Mat 13:35pakuti palibe munthu achita kanthu mobisika...Yoh 7:4ndipo mobisika sindinalankhule kanthu...Yoh 18:20[onaninso:bisalika, chinsinsi, mtseri]

BISIRA (hidden)Yehova wandibisira osandiuza...2 Maf 4:27pobisikira maso a zamoyo...Yob 28:21chilungamo chanu sindinachibisa...Mas 40:10kutsutsika kwanga sikubisikira inu...Mas 69:5ndinawabisa mau anu mumtima...Mas 119:11

BITUNIYA (Bithynia)Mzimu unamuletsa Paulo kupitako...Mac 16:7

Page 20: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

Petro anawalembera akhristu akumeneku...1 Pet 1:1

BOANERGE (Boanerges)dzina la bambo awo a Yakobo ndi Yohane...Marko 3:17

BODZA (lie)kulibe bodza lochokera...1 Yoh 2:21a iwo onena mabodza...1 Tim 4:2[onaninso: nama, namiza, namizira]

BODZA (lying)ndidana nalo bodza...Mas 119:163[onaninso: gona, khala, nama]

BOKOSI (coffin)anamuika iye m’bokosi...Gen 50:26

BOOLA (pierce)mbuye wache amboole khutu lache ndi lisungulu...Eks 21:6

BOWAZI (Boaz)wachuma wokhala ku Betelehemu...Rut 2:1,4-18mwamuna wa Rute...Rut 4:10-13ali mundandanda wa makolo ake a Yesu...Mat 1:5nsanamila ya m’kachisi...1 Maf 7:21

BOZARA (Bozrah)mzinda wa ku Edom...Gen 36:33za kuonongeka kwake zinaneneredwa...Amo 1:12

BUKA (magnified)kosalekeza, abuke Yehova...Mas 35:27[onaninso: kuzidwa]

BUKITSA (magnify)bukitsani pamodzi ndine...Mas 34:3[onaninso: kudzikuza]

BUKU (book)momwemo mudzapeza m’buku...Ezara 4:15nawerenga iwo m’buku...Neh 8:8ha! akadalembedwa m’buku...Yob 19:23funani inu m’buku la Yehova...Yes 34:16lemba m’buku mau onse...Yer 30:2ndi buku la chikumbutso...Mal 3:16zolembedwa m’buku lachilamulo...Agal 3:10Nawaza buku lomwe...Aheb 9:19iwo okha olembedwa m’buku...Chiv 21:27mau a chinenero cha buku...Chiv 22:18akachotsako pa mau a buku...Chiv 22:19

BULU (donkey)bulu uja adaona mngelo...Num 22:23kodi bulu amalira akakhala...Yob 6:5bulu amadziwa kumene mwini...Yes 1:3ndipo yakwera pa bulu...Zek 9:9bulu wake kamwana tsono...Zek 9:9zoonadi yakwera pa kabulu...Mat 21:5adapeza mwana wa bulu...Yoh 12:14bulu, nyama yosalankhula...2 Pet 2:16

BUSA (pasture)nkhosa za busa lanu...Mas 74:1ndife anthu apa busa lake...Mas 95:1ndidzaziwetera kumabusa...Ezek 34:14amandigonetsa pa busa la...Mas 23:2

BUULA (groan)anthu abuula alinkufa...Yob 24:12ifenso tibuula mkati mwathu...Aro 8:23mu msasawu tibuula pothodwa...2 Akor 5:4

BWALO LA MILANDU (court)nkutsutsana ndi Mulungu pa bwalo la milandu...Yob9:19kapananso ndi bwalo lina lililonse la anthu...1 Akor 4:3

BWANYULIDWA (beaten)pochimwa ndi kubwanyulidwapo...1 Pet 2:20[onaninso: kwapula, kwapulidwa, menyedwa]

BWEBWETUKA (babbler)nchiyani afuna kunena wobwebwetuka uyu...Mac 17:18

BWENZI (companion)bwenzi langa wozolowerana naye...Mas 55:13ine ndine bwenzi la anthu...Mas 119:63[onaninso: mnzanga]

BWENZI (friend)monga munthu alankhula ndi bwenzi lake...Eks 33:11mbeu ya Abrahamu bwenzi lanu...2 Mbir 20:7monga ngati iye anali bwenzi langa...Mas 35:14kutali wondikonda ndi bwenzi langa...Mas 88:18bwenzi limakonda nthawi zonse...Miy 17:17liripo bwenzi lipambana ndi mbale...Miy 18:24bwenzi la amisonkho ndi ochimwa...Mat 11:19wa inu adzakhala ndi bwenzi lake...Luk 11:5Lazaro bwenzi lathu ali mtulo...Yoh 11:11amaneyo, simuli bwenzi la Kaisara...Yoh 19:12anatchedwa bwenzi la Mulungu...Yak 2:23amene afuna kukhala bwenzi la dziko...Yak 4:4[onaninso: mnzako]

BWEREKA (lend)bwenzi, ndibwereke mikate...Luk 11:5[onaninso: kongoleta]

BWEZERA (answers)wobwezera mau asanamvetse...Miy 18:13[onaninso: mayankho, vomera]

BWEZERA (avenge)adzabwezera chilango akumuukira...Deut 32:43musabwezere choipa...Aro 12:19kuweruza ndi kubwezera chilango...Chiv 6:10

BWEZERA (avenges)Mulungu wakundibwezera chilango ine...2 Sam 22:48

BWEZERA (reward)andibwezera choipa m’malo mwa chokoma...Mas 35:12kudzaona kubwezera chilango...Mas 91:8ndikuwabwezera machitidwe ao...Hos 4:9[onaninso: landira, mphotho]

BWINJA (desolate)idzasanduka bwinja...Mat 23:38wosanduka bwinja...Chiv 18:19[onaninso: ndekhandekha, wosiyidwa]

BWINO (good)anaona Mulungu kuti kunali kwabwino...Gen 1:10Mulungu anachipangira chabwino...Gen 50:20udawanena ndi abwino...2 Maf 20:19pakuti ankawachitira zabwino...Est 10:3ndani angatiwonetse zabwino...Mas 4:6ndi m’modzi yemwe wochita zabwino...Mas 14:1Chauta ndi wabwino ndi wolungama...Mas 25:8kuti asangalale ndi zinthu zabwino...Mas 34:12Mulungu ndi wabwino kwa olungama...Mas 73:1zinthu zimamuyendera bwino...Mas 112:5Mzimu wanu wabwino...Mas 143:10munthu wabwino amapeza kuyanja...Miy 12:2

Page 21: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mau abwino amamsangalatsa...Miy 12:25amayang’ana oipa ndi abwino omwe...Miy 15:3umakhala ngati mankhwala abwino...Miy 17:22phunzirani kuchita zabwino...Yes 1:17wokalengeza uthenga wabwino...Yes 40:9akubwera ndi uthenga wabwino...Yes 52:7Chauta amuyankha ndi mau abwino...Zek 1:13ataona ntchito zanu zabwino...Mat 5:16munthu wabwino amatulutsa...Mat 12:35ndichite chabwino chanji...Mat 19:16wabwino ndi m’modzi yekha...Mat 19:17wandichitira iyeyuzi ndi zabwino...Mat 26:10ndadzakuuzani uthenga wabwino...Luk 2:10muzichitira zabwino...Luk 6:35ku Nazarete nkuchokera kanthu kabwino...Yoh 1:46kuti, ndi munthutu wabwino...Yoh 7:12ndakuwonetsani ntchito zabwino...Yoh 10:32akuchita ntchito zabwino...Mac 10:38kudzichitira umboni mwa zabwino...Mac 14:17mpaka kufera munthu wabwino...Aro 5:7mwa ine simukhala kanthu kabwino...Aro 7:18gonjetsani zoipa pakuchita zabwino...Aro 12:21ukhale ogwira ntchito zabwino...Aef 2:10pakugwira ntchito zabwino...Akol 1:10kuti malamulo ngabwino...1 Timoteo 1:8zimenezi nzabwino ndi zokondweretsa...1 Tim 2:3kuti azichita zabwino...1 Tim 6:18kugwira ntchito iriyonse yabwino...2 Tim 2:21mphatso iriyonse yabwino...Yak 1:17aziwona ntchito zanu zabwino...1 Pet 2:12zowawa chifukwa chochita zabwino...1 Pet 3:17

BWINO (pleasant)mphamvu yao siiri yabwino...Yer 23:10[onaninso: chofunika, koma, kometsera, kondwera,

kondweretsa]

BWINO (right)ukadachita bwino...Gen 4:7zidzakuyenderani bwino...Deut 4:40zinthu zikumuyendera bwino...Mas 49:18zinthu zidzawayendere bwino...Mlal 8:12zinthu zidzawayendere bwino...Yes 3:10amene ali bwino sasowa...Mat 9:12udachita bwino kwabasi...Mat 25:21otsogolera mpingo bwino...1 Tim 5:17

BWINO (well)ukachita zabwino sudzalandiridwa kodi...Gen 4:7Mulungu naopa pamaso pake adzapeza bwino...Mlal 8:12chabwino, kapolo iwe wabwino ndi wokhulupirika...Mat

25:21akulu akuweruza bwino ayesedwe oyenera...1 Tim 5:17[onaninso:chitsime,koma, komera, limba, ngwiro, pulumutsa]

BZYALA (plant)pali nthawi yobzyala...Mlal 3:2adzabzyala mipesa...Yes 65:21sichinabzyalidwe ndi Atate...Mat 15:13ngati mtengo wobzyalidwa...Mas 1:3mudaubzyala ndi dzanja...Mas 80:15ngati mbeu zobzyala posachedwa...Yes 40:24zuka, kazibzyale...Luk 17:6ineyo ndinabzyala mbeu...1 Akor 3:6wobzyala kapenanso wotsirira...1 Akor 3:7anabzyala tchimo...Yob 4:8ndibzyale ine nadye wina...Yob 31:8sadzabzyala ndipo sadzakolola...Mlal 11:4musabzyale pakati pa minga...Yer 4:3sadzabzyala chakudya...Hos 8:7wobzyala ndi wina...Yoh 4:37wobzyala zochuluka...2 Akor 9:6

zimene munthu amabzyala...Agal 6:7

BZYALA (sow)nabzyala vuto akololapo zomwezo...Yob 4:8ndibzyale ine nadye wina...Yob 31:8inu amene mubzyala m’mbali mwa madzi...Yes 32:20limani masala anu musabzyale paminga...Yer 4:3pakuti abzyala mphepo nadzakolola...Hos 8:7[onaninso: fesa]

BZYALA (sown)mchipululu m’dziko losabzyalamo...Yer 2:2[onaninso: fesa]

C

CHABE (futility)munalengeranji ana onse a anthu kwachabe...Mas 89:47[onaninso: panda pake, utsiru]

CHABE (contemptible)mau ake ndi achabe...2 Akor 10:10[onaninso: nyozeka]

CHACHIKHUMI (tithe)chigawo chachikhumi...Gen 14:20chachikhumi chimene ndakupatsani...Num 18:26chachikhumi muziika padera...Deut 14:22magawo onse a chachikhumi...Deut 14:28muzipereka chopereka chachikhumi...Deut 26:12adzabweranso ndi zachikhumi...2 Mbir 31:5zopereka za chachikhumi...Neh 13:12mumapereka chachikhumi...Mat 23:23

CHACHIKHUMI (tithes)chigawo chimodzi chachikhumi...Lev 27:31zotapa pa chachikhumi...Num 18:28[onaninso: limodzi la magawo khumi]

CHAKA (year)mwezi wanu woyambira chaka...Eks 12:2pa chaka chokondwerera... Lev 27:24ndikalalikire chaka chokomera Yehova ndi tsikulakubwezera...Yes 61:2mpaka pa chaka cha ufulu...Ezek 46:17ku Yerusalemu chaka ndi chaka...Luk 2:41mkulu wansembe yekha kamodzi pachaka...Aheb 9:7kamodzi kokha pa chaka...Aheb 10:3

CHAKUDYA (appetite)ndi kukwaniritsa chakudya cha misona...Yob 38:39[onaninso: dyera]

CHAKUDYA (food)chidzakhala chakudya cha inu...Gen 1:29kuti zikhale chakudya chanu...Gen 9:3ndipo amawapatsa chakudya ndi...Deut 10:18amapereka chakudya chokwanira...Yob 36:31azilima ndikupeza chakudya...Mas 104:14amapatsa zamoyo zonse chakudya...Mas 136:25mumalola chakudya chambiri...Miy 13:23nkuyamba kukonzera chakudya...Miy 31:15kuti akhale chakudya chako...Ezek 4:10mukhale chakudya chambiri...Mal 3:10nkumawagawira chakudya...Mat 24:45inu nkundipatsa chakudya...Mat 25:35amene ali nacho chakudya...Luk 3:11ankadya chakudya chaocho...Mac 2:46pakudya chakudya cha mtundu...Aro 14:15nga chakudya chingaphunthwitse...1 Akor 8:13onse ankadya chakudya chauzimu...1 Akor 10:3ndiponso chakudya choti adye...2 Akor 9:10ngati tiri ndi chakudya ndi zovala...1 Tim 6:8

Page 22: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kukupatsani chakudya cholimba...Aheb 5:12adaagulitsa ukulu wake ndi chakudya...Aheb 12:16ngati chakudya chikhumudwitsa mbale...1 Akor 8:13onse chakudya chauzimu chimodzimodzi...1 Akor 10:3ndi mkate ukhale chakudya, adzapatsa...2 Akor 9:10koma pokhala nazo zakudya ndi zofunda...1 Tim 6:8onga ofuna mkaka osati chakudya chotafuna...Aheb 5:12koma chakudya chotafuna ndicho cha...Aheb 5:14wobadwa nawo mtanda umodzi wa chakudya...Aheb 12:16nichikamsowa chakudya cha tsiku lache...Yak 2:15

CHAKUMWA (drink)uzimpatsa chakumwa chaukali...Miy 31:6nathamangira chakumwa choledzeretsa...Yes 5:11kusakaniza zakumwa zaukali...Yes 5:22kuti akhale chakumwa chako...Ezek 4:11vinyo ndi chakumwa choledzeretsa...Mika 2:11osandipatsa chakumwa...Mat 25:42[onaninso: imwa]

CHALA (finger)olembedwa ndi chala cha...Eks 31:18chala changa chakaninse nchachikulu kuposa chiuno cha...1Maf 12:10mukasiya kulozana chala...Yes 58:9aviike msonga ya chala...Luk 16:24nayamba kulemba pansi ndi chala...Yoh 8:6ika chala chako apa...Yoh 20:27

CHAMPHAMVU (miracle)palibe munthu adzachita champhamvu mdzina langa...Marko9:39[onaninso: chozizwitsa]

CHAM’KAMWA (bit)zomangirira zao ndizo cham’kamwa...Mas 32:9[onaninso: luma]

CHANGU (diligent)tichite changu cha kulowa...Aheb 4:11

CHANGU (zeal)changu cha Chauta...2 Maf 19:21changu changa chikuyaka..Mas 119:139Ine Yehova ndinanena m’changu changa...Ezek 5:13changu chomwe ndinachitira...Yoh 2:17kuti ali ndi changu cha kwa Mulungu...Aro 10:2changu chanu chautsa...2 Akor 9:2[onaninso: nsanje]

CHANGWIRO (faultless)chikadakhala changwiro...Aheb 8:7

CHAPA (washed)adachapa mikanjo yao ndi kuiyeretsa...Chiv 7:14[onaninso: konkha, masula, sambitsa, sambitsidwa, tsuka]

CHAPAFUPI (easier)chapafupi koposa nchiti...Marko 2:9nkwapafupi kuti ngamira...Marko 10:25

CHAUBWEYA (hairy)monga maraya aubweya...Gen 25:25munthu wovala zaubweya...2 Maf 1:8

CHENJERA (beware)chenjera nawoni aneneri onyenga...Mat 7:15chenjerani nawoni ochita zaugaru...Afil 3:2chenjerani kuti wina aliyense...Akol 2:8

CHENJERERA (advantage)satana asatichenjerere...2 Akor 2:11

[onaninso: ubwino]

CHENJEZA (admonish)makamaka mum’chenjeze...2 Ates 3:15[onaninso: langiza]

CHENJEZA (exhort)phunzitse, nuchenjeze...1 Tim 6:2[onaninso: dandaulira]

CHENJEZA (warn)nupanda, kumchenjeza...Ezek 3:18sindidaleka usiku ndi usana kuchenjeza...Mac 20:31koma kuchenjeza inu monga ana...1 Akor 4:14

CHENJEZA (warned)munthu uja adatichenjeza...Gen 43:3Mulungu adawachenjeza...Mat 2:12adakuchenjezani ndani...Mat 3:7Nowa adalandira machenjezo...Aheb 11:7

CHENJEZA (warning)timachenjeza ndi kuphunzitsa...Akol 1:28

CHENJEZEDWA (admonished)mwananga tachenjezedwa... Mlal 12:12

CHEPA (few)nzochepa ndiponso zamavuto...Gen 47:9achepa ndi antchito...Mat 9:37[onaninso: owerengeka]

CHEPETSA (humble)kuti akuchepetseni kukuyesani...Deut 8:2wodzikuza ndi kumchepetsa...Yob 40:11potero dzichepetseni pansi pa dzanja...1 Pet 5:6[onaninso: odzichepetsa, ofatsa, ozunzika, wodzichepetsa,

wofatsa]

CHEPETSA (humbled)nadzichepetsa kwambiri...2 Mbir 33:12anadzichepetsa yekha...Afil 2:8

CHETE (still)adaopa nakhala chete...Mas 76:8ndakhala ndili chete...Yes 42:14[onaninso: bata]

CHEUKA (look)ndi moyo wako usacheuke...Gen 19:17[onaninso: penya, yang’ana]

CHIBADE (skull)chibade cha mutu...Mat 27:33

CHIBADWA (natural)otsutsana ndi achibadwanso...Aro 1:26adaleka makhalidwe a chibadwa...Aro 1:27[onaninso: chibadwidwe]

CHIBADWIDWE (natural)munthu wachibadwidwe...1 Akor 2:14thupi lachibadwidwe...1 Akor 15:44choyamba, koma chachibadwidwe...1 Akor 15:46[onaninso: chibadwa]

CHIBALE (brotherhood)osakumbukira pangano lachibale...Amo 1:9kuti tithetse chibale...Zek 11:14[onaninso: ubale, mbale, abale]

CHIBWANA (foolishness)

Page 23: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

lekani achibwana inu ...Miy 9:6[onaninso: kupusa, opusa, zopusa]

CHIDA (weapon)palibe chida chopangidwa...Yes 54:17akhale atatenga chida...Ezek 9:1

CHIDA CHAPACHIFUWA (breast plate)chachifuwa ndi efodi...Eks 28:4chilungamo monga chida cha pachifuwa...Yes 59:17chapachifuwa cha chilungamo...Aef 6:14

CHIDANI (discord)munthu woutsa chidani...Miy 6:19

CHIDENDENE (heel)iwe udzaluma chidendene...Gen 3:15linali litagwira chidendene...Gen 25:26adandikwezera chidendene chake...Mas 41:9adatsalimira pa ine chidendene chake...Yoh 13:18

CHIDIMA (dim)maso ako adzayamba kuchita chidima...Mlal 12:3[onaninso: mdima]

CHIDZALO (fullness)mwa Iye chikhalira chidzalo...Akol 2:9[onaninso: khuta, kudzala, kudzaza, kwaniridwa,

makwaniridwe]

CHIDZIWITSO (understanding)chidzakhala cha chidziwitso...Mas 49:3koma ndidzayimbanso ndi chidziwitso changa...1 Akor 14:15kulankhula mau asanu ndi chidziwitso...1 Akor 14:19natipatsa ife chidziwitso...1 Yoh 5:20[onaninso: chizindikiritso, kumvera, kuzindikira, luntha, luso,mvetsa, nzeru]

CHIFANIZO (likeness)tipange munthu m’chifanizo chathu...Gen 1:26kapena chifaniziro chiri chonse...Eks 20:4mchifaniziro cha thupi la uchimo...Aro 8:3

CHIFATSO (humility)mphotho ya chifatso...Miy 22:4kudzichepetsa, chifatso...Akol 3:12naonetsere chifatso chonse...Tit 3:2[onaninso: fatsa, kudzichepetsa]

CHIFATSO (gentleness)chifatso chanu chandikuza ine...Mas 18:35mwachikondi ndi mzimu wakufatsa...1 Akor 4:21chifatso, chiletso...Agal 5:23kuonetsera kudzichepetsa konse ndi chifatso...Aef 4:2kufatsa kwanu kuzindikirike...Afil 4:5chikondi, chipiriro, chifatso...1 Tim 6:11

CHIFUKWA (cause)wondisautsa kopanda chifukwa...Mas 7:4okwiya nane kopanda chifukwa...Mas 35:19mbale wake wopanda chifukwa...Mat 5:22anandida ine kopanda chifukwa...Yoh 15:25

CHIFUKWA (complaint)ngati wina ali nacho chifukwa...Akol 3:13[naninso: chifukwa, chitsutsano, kudandaula]

CHIFUNDO (compassion)ndipo adzakuchitirani chifundo...Deut 13:17adzachitira atumiki ake zachifundo...Deut 32:36iye pokhala ngwachifundo...Mas 78:38Ambuye, ndinu Mulungu wachifundo...Mas 86:15

adzawamveranso chifundo...Yer 12:15komabe adzaonetsa chifundo...Mali 3:32chisoni ndi kuchitirana chifundo...Zek 7:9makamu a anthu, adawamvera chifundo...Mat 9:36kuti iwenso umchitire chifundo...Mat 18:33ndikuwamvera chifundo anthuwa...Marko 8:2anene ndifuna kumchitira chifundo...Aro 9:15akhale wokhoza kumva chifundo ndi osadziwa ndiolakwa...Aheb 5:2mukhale a mtima wachifundo...1 Pet 3:8amenewo mudziwachitira chifundo...Yuda 22

CHIFUKWA (fault)ndipo sindinapeza pa munthuyu chifukwa cha zinthuzimene...Luk 23:14[onaninso:cholakwa]

CHIFUNDO (compassionate)ngakhale akazi achifundo...Mali 4:10Ambuye ngachifundo...Yak 5:11chifundo chakenso nchosatha...Mali 3:22

CHIFUNDO (merciful)Mulungu wachifundo ndi wokoma...Eks 34:6tsiku lonse achitira chifundo...Mas 37:26atichitire chifundo Mulungu...Mas 67:1odala ali akuchitira chifundo...Mat 5:7Mulungu mundichitire chifundo...Luk 18:13ndidzachitira chifundo...Aheb 8:12chikondi, ndi wachifundo...Yak 5:11

CHIFUNDO (mercy)ndi kuwachitira chifundo...Eks 20:6wolekereza ndi wachifundo...Num 14:18pakuti chifundo chake...1 Mbir 16:34monga mwa chifundo chanu...Mas 25:7ndikhulupirira chifundo cha...Mas 52:8Mulungu adzatumiza chifundo...Mas 57:3chifundonso ndi chanu...Mas 62:12chifundo chake chalekeka konse konse kodi...Mas 77:8chifundo ndi choonadi...Mas 85:10chifundo adzachimanga kosaleka...Mas 89:2chifundo ndi choonadi zitsogolera...Mas 89:14chifundo chake chimanka muyaya...Mas 100:5ndidzayimba za chifundo...Mas 101:1chifundo chanu nchachikulu...Mas 108:4lidzala nacho chifundo chanu...Mas 119:64kwa Yehova kuli chifundo...Mas 130:7chifundo ndi choonadi...Miy 3:3wochitira wosauka chifundo...Miy 14:31alibe chifundo...Yer 6:23Mulungu wathu ndiye wachifundo...Dan 9:9ndikondwera nacho chifundo...Hos 6:6kukonda chifundo ndi cholinga...Mika 6:8ndifuna chifundo...Mat 9:13chifundo chake chafikira anthu...Luk 1:50ndidzachitira chifundo kwa...Aro 9:15Mulungu amene achitira chifundo...Aro 9:16kuti akachitire onse chifundo...Aro 11:32monga wolandira chifundo kwa...1 Akor 7:25monga talandira chifundo...2 Akor 4:1Mulungu, wolemera chifundo...Aef 2:4komatu anandichitira chifundo...1 Tim 1:13iye apeze chifundo ndi Ambuye...2 Tim 1:18mwa chifundo chake anatipulumutsa...Tit 3:5kuti tilandire chifundo ndi kupeza...Aheb 4:16chiweruziro chiribe chifundo...Yak 2:13ndikulindira chifundo cha Ambuye...Yuda 21

CHIFUNDO (pity)lanu lisawachitire chifundo...Deut 7:16ndichitireni chifundo...Yob 19:21

Page 24: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

wina wondichitira chifundo...Mas 69:20wochitira waumphawi chifundo...Miy 19:17nachitira anthu ake chifundo...Yow 2:18kuchitira chifundo Nineve...Yon 4:11

CHIFUNDO (mercies)chifundo chake nchachikulu...2 Sam 24:14amachitira chifundo za moyo...Mas 145:9a chifundo ndi atilimbitsa mtima...2 Akor 1:3

CHIFUNIRO (will)kapena ku chifuniro cha thupi...Yoh 1:13[onaninso: funa]

CHIFUWA (bosom)mwamuna angatenge moto pa chifuwa...Miy 6:27anatengedwa ndi angelo kunka ku chifuwa...Luk 16:22pachifuwa cha atate...Yoh 13:23mwana wobadwa yekha wakukhala pachifuwa cha Atate...Yoh1:18

CHIFUWA (breast)pachifuwa cha Yesu...Yoh 13:25

CHIFUWA (breasts)ndi kudziguguda pachifuwa...Luk 23:48

CHIGOLOLO (adulterous)Oipa a chigololo...Mat 12:39

CHIGOLOLO (adultery)akachita chigololo...Lev 20:10usachite chigololo...Eks 20:14wochita chigololo...Miy 6:32cha kuchita chigololo...Yer 3:8kuchita naye chigololo...Mat 5:28chifukwa cha chigololo...Mat 5:32achita chigololo...Marko 10:11wogwidwa m’chigololo...Yoh 8:3ndi iwo akuchita chigololo...Chiv 2:22

CHIGUMBU (blade)lidalowa ndi chigumbu chomwe...Ower 3:8

CHIGUMULA (flood)madzi a chigumula anali...Gen 7:10Yehova anakhala pa chigumula...Mas 29:10chisanafike chigumula...Mat 24:38pakulitengera dziko la osapembedza chigumula...2 Pet 2:5[onaninso: madzi akulu]

CHIGWA (valley)ndingakhale ndiyenda m’chigwa...Mas 23:4akamadutsa m’chigwa cha...Mas 84:6maluwa a ku chigwa...Nyi 6:11chigwa chilichonse achidzaze...Yes 40:4pakati pa chigwa...Ezek 37:1dzazani chigwa china...Luk 3:5

CHIKHO (cup)chikho changa chisefuka...Mas 23:5chikho chodzala ndi madzi...Mas 73:10m’dzanja la Yehova muli chikho...Mas 75:8ndidzanyamula chikho cha chipulumutso...Mas 116:13chikho cha ukali wake...Yes 51:17anthu sadzapatsa iwo chikho...Yer 16:7tenga chikho cha vinyo...Yer 25:15chikho cha dzanja la manja la Yehova...Hab 2:16chikho chokha cha madzi...Mat 10:42ndipo pamene anatenga chikho...Mat 26:27chikho ichi chindipitirire...Mat 26:39choteronso chikho atatha m’gonero...Luk 22:20

simungathe kumwera chikho...1 Akor 10:21kuteronso chikho, chitatha chakudya...1 Akor 11:25aupatse chikho cha vinyo...Chiv 16:19[onaninso: chipanda]

CHIKHOMO (peg)natenga chikhomo cha hema...Ower 4:21ndidzamulimbitsa ngati chikhomo...Yes 22:23

CHIKHULULUKIRO (forgiveness)kwa inu kuli chikhululukiro...Mas 130:4kwa inu chikhululukiro cha machimo...Mac 13:38alandire iwo chikhululukiro cha...Mac 26:18chikhululukiro cha zochimwa...Aef 1:7ndiye wachifundo ndi wachifundo ndi wokhululukira...Dan

9:9

CHIKHULUPIRIRO (belief)cha mzimu ndi chikhulupiriro...2 Ates 2:13

CHIKHULUPIRIRO (faith)ana osakhulupirira iwo...Deut 32:20adzakhala ndi moyo mwa chikhulupiriro...Hab 2:4inu akukhulupirira pang’ono...Mat 6:30sindinapeza chikhulupiriro...Mat 8:10chikhulupiriro monga kambeu ka mpiru...Mat 17:20mulibe chikhulupiriro kodi...Marko 4:40khulupirirani Mulungu...Marko 11:22mutionjezere chikhulupiriro...Luk 17:5adzapeza chikhulupiriro...Luk 18:8wodzala ndi chikhulupiriro...Mac 6:5ndi chikhulupiriro cha mwa...Mac 26:18kuti amvere chikhulupiriro...Aro 1:5chakuchokera ku chikhulupiriro...Aro 1:17chichokera mwa chikhulupiriro...Aro 3:28chifukwa cha chikhulupiriro...Aro 3:22chikhulupiriro chake...Aro 4:5pamenepo chikhulupiriro chayesedwa...Aro 4:14a chikhulupiriro cha Abrahamu...Aro 4:16ndiwo mau a chikhulupiriro...Aro 10:8chikhulupiriro chidza ndi mbiri...Aro 10:17umaima ndi chikhulupiriro...Aro 11:20mwa muyeso wa chikhulupiriro...Aro 12:6chikhulupiriro chimene uli nacho...Aro 14:22akudya wopanda chikhulupiriro...Aro 14:23ndingakhale ndiri nacho chikhulupiriro...Akor 13:2tsopano zitsala chikhulupiriro...1 Akor 13:13tiyenda mwa chikhulupiriro...2 Akor 5:7ndiri nao m’chikhulupiriro...Agal 2:20ndikumva kwa chikhulupiriro...Agal 3:2a chikhulupiriro ndiwo ana...Agal 3:7chilamulo sichichokera ku chikhulupiriro...Agal 3:12popeza chadza chikhulupiriro...Agal 3:25komatu chikhulupiriro...Agal 5:6pa banja la chikhulupiriro...Agal 6:10chakuchita mwa chikhulupiriro...Aef 2:8chikhulupiriro chimodzi...Aef 4:5ku umodzi wa chikhulupiriro...Aef 4:13chikopa cha chikhulupiriro...Aef 6:16ntchito yanu ya chikhulupiriro...1 Ates 1:3onse ali nacho chikhulupiriro...2 Ates 3:2kukhala nacho chikhulupiriro...1 Tim 1:19chinsinsi cha chikhulupiriro...1 Tim 3:9wakana chikhulupiriro iye...1 Tim 5:8ndasunga chikhulupiriro...2 Tim 4:7monga mwa chikhulupiriro...Tit 1:4sanasanganizidwa ndi chikhulupiriro...Aheb 4:2koma chikhulupiriro ndicho...Aheb 11:1koma wopanda chikhulupiriro...Aheb 11:6ndiri nacho chikhulupiriro...Yak 2:14iwe uli nacho chikhulupiriro...Yak 2:18osati ndi chikhulupiriro chokha...Yak 2:24

Page 25: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndipo pemphero la chikhulupiriro...Yak 5:15ukoma pa chikhulupiriro...2 Pet 1:5pa chikhulupiriro chanu...Yuda 20pali chipiriro ndi chikhulupiriro...Chiv 13:10ndi chikhulupiriro cha Yesu...Chiv 14:12

CHIKHUMBO (desire)mwampatsa iye chikhumbo...Mas 21:2[onaninso: chilakolako, funitsitsa, khumba, lakalaka]

CHIKHUMUDWITSO (offense)pamenepo chikhumudwitso cha...Agal 5:11[onaninso: chokhumudwitsa, khumudwa,khumudwitsa, lakwa,lakwitsa]

CHIKONDANO (love)tikondwere ndi chikondano...Miy 7:18ngati mulinacho chikondano...Yoh 13:35chikondano chikhale chopambana...Aro 12:9chikondano sichichitira mnzake...Aro 13:10mukhale nacho chikondano chenicheni...1 Pet 4:8[onaninso: chikondi, konda, kondana, kukondana]

CHIKONDI (affection)chikondi chake...Afil 2:1[onaninso: konda]

CHIKONDI (love)chikondi chako ndinadadwa nacho...2 Sam 1:26koma chikondi chikwirira zolakwa...Miy 10:12chikondi chake chiposa...Nyi 1:2yondizolimira inali yachikondi...Nyi 2:4ngakhale kugalamutsa chikondi...Nyi 3:5pompo ndidzakupatsa chikondi...Nyi 7:12chikondi chilimba ngati ufa...Nyi 8:6mulibe chikondi cha Mulungu...Yoh 5:42munthu alinacho chikondi choposa...Yoh 15:13chifukwa chikondi cha Mulungu...Aro 5:5koma chikondi chimangirira...1 Akor 8:1chikondi chikhala chilezere...1 Akor 13:4chikondi sichidukidwa...1 Akor 13:4chikondi sichidziwa kudzitama...1Akor 13:4chikondi sichitha nthawi zonse...1 Akor 13:8chachikulu cha izi ndicho chikondi...1 Akor 13:13chikondi cha Khristu chitikakamiza...2 Akor 5:14Mulungu wa chikondi ndi mtendere...2 Akor 13:11ndicho chikondi, chimwemwe...Agal 5:22mu ufumu wa mwana wa chikondi...Akol 1:13cha chilamulo ndicho chikondi...1 Tim 1:5m’chikhulupiriro ndi chikondi...1Tim 2:15m’mayendedwe, mchikondi...1Tim 4:12ndiwo chikondi cha pa ndalama...1Tim 6:10chikondi cha pa abale...Aheb 13:1ndi chipsopsono cha chikondi...1 Pet 5:14pachipembedzo chikondi cha pa...2 Pet 1:7umo tizindikira chikondi...1Yoh 3:16nanga chikondi cha Mulungu...1Yoh 3:17umo muli chikondi, sikuti...1Yoh 4:10m’menemo chikondi chathu chikhala...1Yoh 4:17pakuti ichi ndi chikondi cha Mulungu...1Yoh 5:3unataya chikondi chako...Chiv 2:4[onaninso: chikondano, konda, kondana, kukondana]

CHIKONDI (lovingkindness)za chikondi chanu chosasinthika...Mas 40:10chifukwa chikondi chanu nchabwino...Mas 63:3kulalika za chikondi chanu...Mas 92:2chikondi chopanda malire...Yer 31:3

CHIKONDWERERO (dancing)munandiveka chikondwerero...Mas 30:11[onaninso: kuvina]

CHIKONDWERERO (delight)m’chilamulo cha Yehova muli chokondwerero...Mas 1:2kuchita chikondwerero chanu...Mas 40:8kukhala chikondwerero changa...Mas 119:92[onaninso: kwezeka,sekeretsa]

CHIKONDWERERO (feast)mumaitanidwa ku chikondwerero...Mali 2:22masiku anu a chikondwerero...Amo 5:21chaka cha chikondwerero...Luk 2:41chikondwerero chija cha...Yoh 6:4tsiku lotsiriza la chisangalalo...Yoh 7:37tsono, tichite chikondwerero...1 Akor 5:8[onaninso: phwando, madyerero]

CHIKONDWERERO (gladness)tumikirani Yehova ndi chikondwerero...Mas 100:2[onaninso: kukondwera]

CHIKUMBUKIRO (memorial)chidzakambidwanso chikumbukiro...Mat 26:13chidzanenedwa chikhale chomkumbukira...Marko 14:9chikumbukiro chake chidzatayika...Yob 18:17kuti adule chikumbukiro chao...Mas 109:15wodala pomkumbukira...Miy 10:7

CHIKUMBUMTIMA (conscience)chikumbumtima chosanditsutsa...Mac 24:16chikumbumtima changa chichita umboni...Aro 9:1komanso chifukwa cha chikumbumtima...Aro 13:5osafunsa kanthu chifukwa cha chikumbumtima...1 Akor 10:25m’chikumbumtima choona...1 Tim 3:9olotchedwa m’chikumbumtima mwao...1 Tim 4:2udzayeretsa chikumbumtima chanu...Aheb 9:14kuichotsera chikumbumtima choipa...Aheb 10:22ndikukhala nacho chikumbumtima chabwino...1 Pet 3:16

CHIKWERE (cage)monga chikwere chodzala ndi mbalame...Yer 5:27

CHILAKOLAKO (desire)chilakolako chimachita ngati chatenga...Yak 1:15[onaninso: chikhumbo, funitsitsa, khumba, lakalaka]

CHILALA (drought)m’dziko la chilala ndi la...Yer 2:6pa chaka cha chilala sakuda...Yer 17:8ndagwetsa chilala padziko lonse...Hagai 1:11

CHILAMULO (decree)anadzipatsanso chilamulo chosatumphika...Mas 148:6[onaninso: chitsimikizo, lamulo]

CHILAMULO (law)chitsanzo cha chilamulo cha Mose...Yos 8:32ndikondwera nacho chilamulo...Mas 119:70chilamulo cha pakamwa panu...Mas 119:72chilamulo chanu chindikondweretsa...Mas 119:77ndikondadi chilamulo chanu...Mas 119:97chilamulo chanu ndicho choona...Mas 119:142chilamulo cha zoona chinali...Malak 2:6amitundu akuswa chilamulo...Mali 2:9M’ziyoni mudzatuluka chilamulo...Yes 2:3ndinadza ine kudzapasula chilamulo...Mat 5:17pakuti ichi ndicho chilamulo...Mat 7:12mpokoloweka chilamulo chonse...Mat 22:40chilamulo ndi aneneri alipo...Luk 16:16chilamulo chinapatsidwa mwa Mose...Yoh 1:17chilamulo chathu chiweruza munthu...Yoh 7:51kodi chilamulo chiri uchimo...Aro 7:7chilamulo chiri chauzimu...Aro 7:14

Page 26: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: lamulo]

CHILANGIZO (instruction)chilangizo cha mchilungamo...2 Tim 3:16[onaninso: langiza, malangizo, mwambo]

CHILANGO (punishment)chilango chimenechi nchopitirira...Gen 4:13mudzatani patsiku la chilango...Yes 10:3tsiku limene ndidzawalanga...Yer 8:12pamene anthuwo adzalangidwe...Yer 10:15pamene alangidwa chifukwa cha...Mali 4:39chilango cha anthu anga...Mali 4:6nthawi ya chilango yafikadi...Hos 9:7sindileka kulanga...Amo 1:3kumapita ku chilango chosatha...Mat 25:46choncho chilangocho nchokwanira...2 Akor 2:6chilango cha munthu wotere...Aheb 10:29zizilanga ochita zoipa...1 Pet 2:14osalungama kuti alangidwe...2 Pet 2:9

CHILANGO (condemnation)Mulungu adzakulangani koposa...Mat 23:14mudzachipewa bwanji chilango...Mat 23:33[onaninso: chitsutso, chiweruzo]

CHILEMA (blemish)yopanda chilema...Lev 6:6woyera ndi wopanda chilema...Aef 5:27wopanda chilema...1 Pet 1:19

CHILEMA (defect)wakukhala nacho chilema...Lev 21:17

CHILEMA (spot)ulibe nkachilema komwe...Nyi 4:7nsembe yopanda chilema...Aheb 9:14lopanda banga, lopanda chilema...1 Tim 6:14[onaninso: banga]

CHILENDO (strange)anawayesa achilendo...Hos 8:12mukutiwuzazi nzachilendo...Mac 17:20mmenemo ayesa nchachilendo kuti simuthamanga...1 Pet 4:4ngati chinthu chachilendo chachitika nanu...1 Pet 4:12[onaninso: zodabwitsa]

CHILENGEDWE (creation)kuyambira chiyambi cha chilengedwe...Marko 13:19tidziwa kuti chilengedwe chonse...Aro 8:22wobadwa woyamba wa chilengedwe...Akol 1:15[onaninso: cholengedwa, wolengedwa]

CHILIMBANO (conflict)ndi kukhala nacho inu chilimbano...Afil 1:30[onaninso: nkhawa]

CHILIMBIKITSO (boldness)pokhala nacho chilimbikitso...Aheb 10:19[onaninso: kulimbika]

CHILIMWE (summer)malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku...Gen 8:22unasanduka kuuma kwa malimwe...Mas 32:4mudakhazikitsa chilimwe...Mas 74:17pa nthawi ya chilimwe...Zek 14:8[onaninso: dzinja]

CHILUNGAMO (righteous)ndi dzanja langa lamanja lachilungamo...Yes 41:10dulani machimo anu ndi kuchita chilungamo...Dan 4:27[onaninso: olungama, wolungama, zolungama]

CHILUNGAMO (righteousness)mumakonda chilungamo...Mas 45:7chilungamo cha Mulungu...Mas 50:6chilungamo ndi mtendere...Mas 85:10chilungamo chidzabwereranso...Mas 94:15chilungamo chimpulumutsa...Miy 10:2wofunitsitsa chilungamo...Miy 11:19njira ya chilungamo imafikitsa...Miy 12:28chilungamo chimatchinjiriza...Miy 13:6chilungamo chimakweza mtundu...Miy 14:34amene amapatsa chilungamo...Miy 21:21wokhulupirika ndi wachilungamo...Yes 1:21adzawaweruza mwa chilungamo...Yes 11:4chilungamo chidzakhala ngati...Yes 11:5saphunzira zachilungamo...Yes 26:10chilungamo ndicho chidzakhala...Yes 28:17onse akamachita zachilungamo...Yes 32:17chilungamo ndiponso mphamvu...Yes 45:24adavala chilungamo...Yes 59:17mitengo ya mphamvu ya chilungamo...Yes 62:1Chauta ndi chilungamo chathu...Yer 23:6chilungamo cha muyaya chidzafika...Dan 9:24m’njira ya chilungamo adzawala...Dan 12:3mudzifetsere m’chilungamo...Hos 10:12njira ya chilungamo...Mat 21:32pamodzi ndi chilungamo...Aro 5:17kulamulira pakudzetsa chilungamo...Aro 5:21osagonjera chilungamo chochokera...Aro 10:3valani chilungamo ngati...Aef 6:14mtima wofuna chilungamo...1 Tim 6:11nalandira chilungamo chimene...Aheb 11:7safikapo pa chilungamo...Yak 1:20zowawa chifukwa cha chilungamo...1 Pet 3:14mlaliki wa chilungamo...2 Pet 2:5m’mene chilungamo chidzakhalamo...2 Pet 3:13aliyense wochita chilungamo...1 Yoh 2:29amene amachita chilungamo...1 Yoh 3:7aliyense wochita chilungamo...1 Yoh 3:10

CHIMALIZO (end)nthawi ya chimalizo...Amo 8:2chimalizo chija chafika kale...Mat 24:6anawakonda kufikira chimaliziro...Yoh 13:1Khristu ali chimaliziro cha...Aro 10:4chimalizo cha zonse cha...1 Pet 4:7[onaninso: chitsiriziro, itha, maliza, mathero, matsiriziro,

tsiriza]

CHIMANJAMANJA (empty)pamaso panga ali chimanjamanja...Eks 23:15

CHIMASULIRO (interpretation)ali nacho chimasuliro...1 Akor 14:26[onaninso: tanthauzo]

CHIMODZIMODZI (alike)zigwera onse chimodzimodzi...Mlal 9:2

CHIMWA (sin)ndipo musachimwe...Mas 4:4ndisachimwe polankhula...Mas 39:1kuchimwa kwanga...Mas 51:3osachimwa konse...Mlal 7:20masiku ano akuchimwirachimwira...Hos 13:2aliyense wochimwitsa...Mat 18:6tsopano, usakachimwenso...Yoh 5:14amene sadachimwepo...Yoh 8:7pa za kuchimwa...Yoh 16:8onse ndi ochimwa...Aro 3:9Khristu sadachimwe...2 Akor 5:21koma iye sadachimwepo...Aheb 4:15

Page 27: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

tikamachimwirachimwira mwadala...Aheb 10:26ndiye kuti wachimwa...Yak 4:17zimenezi kuti musamachimwa...1Yoh 2:1aliyense amene amachimwa...1 Yoh 3:4[onaninso: tchimo, uchimo]

CHIMWA (sinful)ndi ochimwa kwambiri pamaso pa Yehova...Gen 13:13gulu la anthu ochimwa kuonjezamo mkwiyo...Num...32:14mtundu wochimwa inu, anthu olemedwa ndi mphulupulu...Yes1:4maso a Ambuye Yehova alu pa ufumu wochimwa...Amo 9:8mu mbadwo uno wachigololo ndi wochimwa...Marko 8:38muchoke kwa ine Ambuye chifukwa ndine munthuwochimwa...Luk 5:8ayenera kuperekedwa m’manja a anthu ochimwa...Luk 24:7zilakolako za machimo zimene zinali mwa chilamulo...Aro 7:5kuti uchimo ukhale wochimwitsa ndithu mwa lamulo...Aro

7:13Iye yekha m’chifanizo cha thupi la uchimo...Aro 8:3

CHIMWA (sinned)ndachimwira inu...Mas 51:4Yerusalemu adachimwa...Mali 1:8makolo athu adachimwa...Mali 5:7ndidachimwira Mulungu...Luk 15:18kodi adachimwa ndani...Yoh 9:2onse amene adachimwa...Aro 2:12kuti onse adachimwa...Aro 3:23ukwatira, sukuchimwa ai...1 Akor 7:28kuti sitidachimwe...1 Yoh 1:10saatana ndi wochimwa...1 Yoh 3:8

CHIMWEMWE (rejoicing)chiyembekezo chathu kapena chimwemwe...1 Ates 2:19[onaninso: kondwera, kudzitamandira]

CHINENERO (prophecy)ndi kwa wina chinenero...1 Akor 12:10chinenero sichinadza ndi chifuniro...2 Pet 1:21wa Yesu ndiwo Mzimu wa chinenero...Chiv 19:10akachotsa pa mau a buku la chinenero...Chiv 22:19

CHINGALAWA (ark)m’kukonzeka chingalawa...1 Pet 3:20[onaninso: chombo, likasa la pangano]

CHINGWE (cord)chingwe ichi chofiira...Yos 2:18ndipo chingwe cha nkhosi...Mlal 4:12chingwe cha siliva chisanaduke...Mlal 12:6

CHINGWE (line)chingwe cholungamitsira chiriri...Amo 7:8[onaninso: muyeso, mzere]

CHINJIRIZA (defend)pakuti ndidzachinjiriza mudzi uno kupulumutsa...2 Maf 19:34ndidzachinjiriza mudzi uno chifukwa cha Ine ndekha...2 Maf20:6Inu muwachinjirize kuti okukondani akondwere...Mas 5:11sachinjiriza ana amasiye ndipo samvera madandaulo...Yes

1:23Yehova wamakamu adzachinjiriza mzinda wa

Yerusalemu...Yes31:5pakuti ndidzachinjiriza mudzi uno, kuupulumutsa...Yes 37:35ndipo ndidzachinjiriza mudzi uno...Yes 38:6Yehova wamakamu adzawachinjiriza...Zek 9:15Tsiku ilo Yehova adzachinjiriza okhala mu Yerusalemu...Zek12:8malo ake ochinjirizika...Yes 33:16

[onaninso: teteza, umirira]

CHINJOKA (dragon)chinjoka chachikuru, chofiira...Chiv 12:3kumenyana ndi chinjoka...Chiv 12:7adachipembedza chinjoka chija...Chiv 13:4adagwira chinjoka chija...Chiv 20:2

CHINKHUPULE (sponge)nakatenga chinkhupule...Mat 27:48

CHINSIKWI (blight)ndinakukanthani ndi chinsinkwi...Amo 4:9ndinakukanthani ndi chinsinkwi...Hagai 2:17

CHINSINSI (mystery)chinsinsi cha ufumu wa Mulungu...Marko 4:11nzeru ya Mulungu m’chinsinsi...1 Akor 2:7taonani ndikuuzani chinsinsi...1 Akor 15:51anatizindikiritsa ife chinsinsi...Aef 1:9chinsinsi ichi nchachikulu...Aef 5:32ndiwo chinsinsicho chobisika...Akol 1:26chinsinsi chakuchitira Mulungu...1 Tim 3:16

CHINSINSI (secret)zinsinsi nza Yehova Mulungu wathu, komazovumbuluka...Deut 19:19ndili nao mau a chinsinsi kwa inu mfumu...Owe 3:19chinsinsi cha mphamvu yakeyo sichinadziwike...Ower 16:9chinsinsi cha Yehova chili pa iwo akumuopa Iye...Mas25:14ndibiseni pa upo wachinsinsi wa ochita zoipa...Mas 64:4pamene ndinkapangidwa mwachinsinsi...Mas 139:15koma chinsinsi chake chili pa oongoka...Miy 3:32zoipa ngakhale ndi zachinsinsi zonse...Mlal 12:14palibe chinsinsi angakubisire...Ezek 28:3kwa Mulungu wakumwamba pa chinsinsi ichi...Dan 2:18chinsinsicho chinavumbulitsidwa kwa Danieli...Dan 2:19chinsinsi inachitira liuma mfumu...Dan 2:27koma ine chinsinsi ichi sichinavumbulutsidwe...Dan 2:30popeza wakhonza kuvumbulutsa chinsinsi...Dan 2:47ndi kuti palibe chinsinsi chakusautsa...Dan 4:9kapena chinsinsi chimene sichidziwika...Luk 8:17monga mwa vumbulutso la chinsinsi...Aro 16:25

CHINTHENDA (burden)akadziwa yense chinthenda chake...2 Mbir 6:29[onaninso: katundu, kukoka, lemetsa, nkhawa]

CHINYANSO (lewdness)masiriro, zoipa, chinyengo, chinyanso...Marko 7:22si m’chigololo ndi chonyansa...Aro 13:13okha kuti akakhumbe zonyansa...Aef 4:19poyendayenda ife m’kukhumba zonyansa...1 Pet 4:3

CHINYENGO (deceit)mumzimu mwake mulibe chinyengo...Mas 32:2milomo yako isalakhule chinyengo...Mas 34:13wakuchita chinyengo sadzakhala...Mas 101:7chinyengo chiri m’mitima ya oganizira...Miy 12:20mkamwa mwako mulibe chinyengo...Yes 53:9agwiritsa chinyengo, akana kubwera...Yer 8:5mwa iye mulibe chinyengo...Yoh 1:47wodzala ndi chinyengo...Mac 13:10ndi chinyengo chopanda pake...Akol 2:8mkamwa mwake sichinapezeka chinyengo...1 Pet 2:22ndi chinyego cha chuma...Mat 13:22

CHIONONGEKO (pit)munandikwezera moyo wanga kuuchotsa ku

Page 28: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

chionongeko...Yon 2:6[onaninso: dzenje, manda, phompho]

CHIONONGEKO (perdition)chisonyezo cha chionongeko...Afil 1:28mwana wa chionongeko...2 Ates 2:3akubwerera kulowa chionongeko...Aheb. 10:39la chiweruzo ndi chionongeko...2 Pet 3:7

CHIPALE CHOFEWA (snow)chilala ndi dzuwa zitha madzi a chipale chofewa...Yob 24:19pakuti anena kwa chipale chofewa...Yob 37:6kodi unalowamo m’zosungiramo chipale chofewa...Yob 38:22apatsa chipale chofewa ngati ubweya...Mas 147:16monga chipale chofewa m’malimwe...Miy 26:1saopera banja lake chipale chofewa...Miy 31:21zinali za mbu ngati chipale chofewa...Dan 7:9ubweya woyera ngati chipale chofewa...Chiv 1:14[onaninso: matalala]

CHIPANDA (cup)Yerusalemu akhale chipanda...Zek 12:2[onaninso: chikho]

CHIPANGANO (convenant)Yehova anapangana chipangano...Gen 15:18kumbukirani chipangano chake...1 Mbir 16:15ndipo chipangano changa...Mas 89:28ana ako akasunga chipangano...Mas 132:12tidachita chipangano...Yes 28:15adzachita chipangano...Dan 11:6ndi mthenga wa chipangano...Mal 3:1nkhoswe ya chipangano chatsopano...Aheb 12:24ndi mwazi wa chipangano...Aheb 13:20[onaninso: pangano]

CHIPATA (gate)chipata cha Yehova ndi ichi ...Mas 118:20lowani pa chipata chopapatiza ...Mat 7:13pa chipata cha nkhosa...Yoh 5:2chowawa kunja kwa chipata...Aheb 13:12

CHIPATSO (fruit)wakupatsa chipatso chake...Mas 1:3chipatso changa chiposa golide...Miy 8:19chipatso cha wolungama ndi mtengo...Miy 11:30ndilenga chipatso cha milomo...Yes 57:19sindidzadyanso chipatso ichi...Mat 26:29chodalitsika chipatso cha mimba...Luk 1:42anadza nafuna chipatso pa uwu...Luk 13:6ngati udzabala chipatso...Luk 13:9ndi iriyonse yakubala chipatso...Yoh 15:2kuti mubale chipatso chambiri...Yoh 15:8mukamuke inu ndi kubala chipatso...Yoh 15:16chipatso cha mzimu ndicho...Agalatiya 5:22nditsata chipatso chakuchulukira...Afil 4:17chipatso cha chilungamo chifesedwa...Yak 3:18[onaninso: zipatso]

CHIPEMBEDZERO (religion)a chipembedzero cha iwo okha...Mac 25:19[onaninso: kupembedza, mapembedzedwe, wopembedza]

CHIPEMBEDZO (religion)ankangokangana naye za chipembedzo...Mac 25:19chipembedzo chakecho nchopanda...Yak 1:26chipembedzo choona ndi changwiro...Yak 1:27

CHIPHAMASO (hypocrisy)m’modzadza ndi chiphamaso...Mat 23:28chimene chiri chiphamaso...Luk 12:1chizikhala chopanda chiphamaso...Aro 12:9

adayamba kuchita chiphamaso...Agal 2:13kapena kuchita chiphamaso...Yak 3:17kunyenga konse, chiphamaso...1 Pet 2:1adaatengeka nacho chiphamaso...Agal 2:13

CHIPHUNZITSO (doctrine)unena, chiphunzitso changa nchoona...Yob 11:4pakuti ndakuphunzitsani...Miy 4:2cha mikate, koma chiphunzitso...Mat 16:12nchiyani? Chiphunzitso chatsopano...Marko 1:27

CHIPHUNZITSO (teaching)chiphunzitso changa sichiri changa...Yoh 7:16Yerusalemu ndi chiphunzitso chanu...Mac 5:28makhalidwe aja a chiphunzitso...Aro 6:17ndi mphepo yonse ya chiphunzitso...Aef 4:14kakutsutsana nacho chiphunzitso...1 Tim 1:10watsatsata chiphunzitso changa...2 Tim 3:10lipindulitsa pa chiphunzitso...2 Tim 3:16sadzalola chiphunzitso...2 Tim 4:3m’chiphunzitso chako uonetsere...Tit 2:7akakometsere chiphunzitso cha ...Tit 2:10wosakhala m’chiphunzitso cha Khristu...3 Yoh 9

CHIPHUPHU (bribe)usalandire chiphuphu...Eks 23:8asadzalandire chiphuphu...Deut 16:19kulandira chiphuphu kumaononga...Mlal 7:7aliyense amakonda chiphuphu...Yes 1:23[onaninso: ziphuphu]

CHIPINDA (room)adzakusonyezani chipinda...Marko 14:15anakwera ku chipinda...Mac 1:13[onaninso: malo]

CHIPIRIRO (endurance)pakuti chikusowani chipiriro...Aheb 10:36ndipo tithamange mwachipiriro...Aheb 12:1

CHIPIRIRO (patience)Mulungu wa chipiriro...Aro 15:5ndi chipiriro cha chiyembekezo...1 Ates 1:3chikhulupiriro, chikondi, chipiriro...1 Tim 6:11chikhulupiriro chanu chichitira chipiriro...Yak 1:3chipiriro chikhale nayo ntchito...Yak 1:4ufumu ndi chipiriro zokhala...Chiv 1:9pali chipiriro ndi chikhulupiriro...Chiv 13:10[onaninso: kuleza mtima, kupirira]

CHIPIRIRO (longsuffering)ndi kuonetsera chipiriro...Aef 4:2chipiriro chonse ndi kuleza mtima...Akol 1:11[onaninso: kuleza mtima, kusapsa mtima msanga]

CHIPIRIRO (perseverance)chisautso chichita chipiriro...Aro 5:3kulezamtima, chikondi, chipiriro...2 Tim 3:10pa chodziletsa chipiriro...2 Pet 1:6

CHIPIRIRO (persevere)unasunga mau a chipiriro...Chiv 3:10

CHIPOLOWE (disorderly)mlandu wochita chipolowe...Mac 19:40[onaninso: dwachedwache]

CHIPSINJO (anguish)ndi chipsinjo zimchititsa mantha...Yob 15:21[onaninso: kusauka, kusautsika, kuwawa mtima, nkhawa]

CHIPULULU (desert)

Page 29: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

chipululu ndi malo ouma...Yes 35:1ndidzakonzadi njira m’chipululu...Yes 43:19kunka kumalo a chipululu...Mat 14:13onani iye ali m’chipululu, musamukeko...Mat 24:226

CHIPULULU (wilderness)adawapeza mchipululu...Deut 32:10ku chipululu ngati mbidzi...Yob 24:5chikutulukira ku chipululu...Nyi 3:6chipululu ndi kugwetsa mizinda...Yes 14:17ndidzasandutsa chipululu kukhala...Yes 42:11ndakhala ngati chipululu...Yer 2:31munthu wofuula m’chipululu...Mat 3:3njoka pamtengo m’chipululu...Yoh 3:14msonkhano wa Israeli m’chipululu...Mac 7:38ndidzasandutsa chipululu chikhale...Yes 41:18

CHIPULULUTSO (desolation)chonyansa chakupululutsa...Mat 24:15chipululutso chake chayandikira...Luk 21:20[onaninso: zopululutsa]

CHIPULUMUTSO (deliverance)mfumu yake ndi chipulumutso...Mas 18:50koma wopulumutsa ndiye Yehova...Miy 21:31[onaninso: kuomboledwa]

CHIPUPA (wall)chipupa chopaka njeresawe...Mac 23:3

CHIRANGALI (flame)anamuonekera m’chirangali ha moto...Eks 3:2[onaninso: lawi, lilime, malawi]

CHIRIKIZA (uphold)mundichirikize monga mwa mau...Mas 119:116ndinadabwa kuti panalibe wochirikiza...Yes 63:5[onaninso: gwirizitsa, sankhula]

CHIRITSA (cure)koma iwo sanathe kumchiritsa...Mat 17:16ndadzakuchiritsa thenda, ...Luk 9:1

CHIROMBO (beast)wajiwa ndi chirombo...Gen 37:20ndipo ndinaona chirombo ...Chiv 13:1ndipo ndinaona chirombo china...Chiv 13:11ndipo ndinaona chirombocho...Chiv 19:19ndipo chinagwidwa chirombocho...Chiv 19:20

CHISA (nest)kukamanga chisa pamwamba...Yob 39:27yosokera kutali ndi chisa...Miy 27:8ngakhale mumange chisa...Obad 4[onaninso: chisanja]

CHISAKASA (lute)galamuka, chisakasa ndi zeze...Mas 57:8ndidzakuyamikani ndi chisakasa...Mas 71:22wokondwetsa pamodzi ndi chisakasa...Mas 81:2cha zingwe khumi ndi chisakasa...Mas 92:3galamukani, chisakasa ndi zeze...Mas 108:2mlemekezeni ndi chisakasa ndi zeze...Mas 150:3

CHISALUNGAMO (injustice)wopanda chisalungamo...Deut 32:4chosalungama chanji mwa ine...Yer 2:5[onaninso: oipa]

CHISANDULIKO (conversion)nafotokozera chisanduliko cha...Mac 15:3

CHISANGALATSO (consolation)mwalandira chisangalatso chanu...Luk 6:24anatipatsa chisangalatso chosatha...2 Ates 2:16[onaninso: chitonthozo]

CHISANJA (nest)kuti aike chisanja chake ponyamuka...Hab 2:9[onaninso: chisa]

CHISANKHO (election)koma kunena za chisankho...Aro 11:28

CHISANU (cold)chisanu ndi mafundi...Gen 8:22[onaninso: zilala, zizira]

CHISAUKO (distress)chisauko cha mitundu ya anthu...Luk 21:25[onaninso: chivuto, mavuto, nsauko, nsautso, opsa, psinjika,

saukira, sautsika]

CHISAUTSO (affliction)pakuti chisautso chathu chopepuka...2 Akor 4:17chisautso mzomangira zanga...Afil 1:16mauwo m’chisautso chambiri...1 Ates 1:6[onaninso: kuthyoka, kuzunza, kuzunzika, masautso, mazunzo,

nsauko, nthenda]

CHISHANGO (shield)ngati chishango chako...Gen 15:1iye ndiye chishango...2 Sam 22:31ndiye chishango changa...Mas 18:2dzuwa ndi chishango...Mas 84:11kumateteza monga chishango...Mas 91:4ngati chishango chanu...Aef 6:16

CHISIRIRO (covetousness)koma yemwe ada chisiriro...Miy 28:16chidetso chonse, kapena chisiriro...Aef 5:3[onaninso: sirira, msiriro, kangamira]

CHISOMO (beauty)yina ndinaitcha chisomo...Zek 11:7[onaninso: chisomo, koma, kongoletsa,kukongola, ulemelero]

CHISOMO (favor)ndi m’chisomo cha pa Mulungu...Luk 2:52[onaninso: komera mtima, konda, kukoma mtima]

CHISOMO (grace)anakutsanulirani chisomo...Mas 45:2Mzimu wa chisomo ndi wakupembedza...Zek 12:10ndi chisomo cha Mulungu chinali...Luk 2:40chisomo ndi choonadi zinadza...Yoh 1:17panali chisomo chachikulu pa iwo...Mac 4:33chisomo chikhale ndinu...Aro 1:7kuchuluka kwake kwa chisomo...Aro 5:17koma ngati kuli ndi chisomo...Aro 11:6chisomo cha Ambuye wathu...Aro 16:20mudziwa chisomo cha Ambuye wathu...2 Akor 12:9chisomo cha Ambuye Yesu Khristu...2 Akor 13:14mudagwa posiyana nacho chisomo...Agal 5:4monga mwa kulemera kwa chisomo...Aef 1:7muli opulumutsidwa ndi chisomo...Aef 2:8za udindo wa chisomo cha...Aef 3:2kwa yense wa ife kwapatsidwa chisomo...Aef 4:7akhale nacho chisomo onse...Aef 6:24tikhale nacho chisomo...Aheb 12:28koma apatsa chisomo choposa...Yak 4:6chisomo choona cha Mulungu ndi ichi...1 Pet 5:12kulani m’chisomo ndi chizindikiritso...2 Pet 3:18[onaninso: ufulu]

Page 30: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

CHISONI (grief)chinthenda chake ndi chisoni...2 Mbir 6:29atayesa bwino chisoni changa...Yob 6:2ndinena chisoni changa sichitsika...Yob 16:6mumayang’anira chivutitso ndi chisoni...Mas 10:14matsiriziro a chiphwete ndi chisoni...Miy 14:13m’nzeru yambiri muli chisoni...Mlal 1:18ndi chimwemwe, osati mwachisoni...Aheb 13:17[onaninso: zowawa]

CHISONI (mourn)odala ali achisoni chifukwa...Mat 5:4[onaninso: kulira mokuwa]

CHISONI (pity)ndi mchisoni chake Iye adawaombola...Yes 63:9monga inenso ndinakuchitira iwe chisoni?...Mat 18:33

CHISONI (sorrow)pokhala ndi chisoni...Mas 13:2chisoni changa chili pamaso...Mas 38:17ndinapeza nsautso ndi chisoni...Mas 116:3alemeretsa, saonjezerapo chisoni...Miy 10:22a chiphwete ndi chisoni...Miy 14:13chisoni chiposa kuseka...Mlal 7:3la kulira ndi la chisoni...Yes 17:11mudzalira ndi mtima wa chisoni...Yes 65:14kodi ndidabadwira mavuto ndi chisoni...Yer 20:18Yehova waonjezera chisoni...Yer 45:3nawapeza ali m’tulo ndi chisoni...Luk 22:45chisoni chadzala mumtima...Yoh 16:6mudzachita chisoni inu...Yoh 16:20ndagwidwa ndi chisoni...Aro 9:2chisoni cha kwa Mulungu...2 Akor 7:10ndisakhale nacho chisoni...Afil 2:27kuti chisoni chanu chisakhale ngati cha...1 Ates 4:13sipadzakhalanso imfa, chisoni, kulira kapena...Chiv 21:4[onaninso: mantha, kulira, kupweteka, kusauka]

CHISONI (sorrowful)iwo anali ndi chisoni...Mat 17:23wozingidwa ndi chisoni...Mat 26:38chisoni chanu chidzasandulika...Yoh 16:20amene ndamvetsa chisoni...2 Akor 2:2inenso chindichepere chisoni...Afil 2:28[onaninso: wachisoni, zisoni, zowawa]

CHISONI (torment)mudzagona pansi ndi chisoni...Yes 50:11[onaninso: zunza]

CHISOTI (helmet)kumutu kwake adavala chisoti...Yes 59:17landirani chipulumutso ngati chisoti...Aef 6:17ngati chisoti choteteza kumutu...1 Ates 5:8

CHISOTI (diadem)udzakhala ngati chisoti chaufumu...Yes 62:3chitavala chisoti chaufumu...Chiv 12:3

CHITA DZIMBIRI (corroded)ndi siliva wanu zachita dzimbiri...Yak 5:3

CHITA MANYAZI (ashamed)ndi kuchita manyazi kuweramutsa nkhope ...Ezara 9:6adzachita manyazi, nadzanthunthumira...Mas 6:10ndisachite manyazi...Mas 25:2sadzachita manyazi...Mas 25:3anzeru ali ndi manyazi...Yer 8:9adzakhala ndi manyazi...Yer 17:13Israeli adzachita manyazi...Hos 10:6

yense wakuchita manyazi...Marko 8:38uthenga wabwino sundichititsa manyazi...Aro 1:16palibe chinthu chidzandichititsa manyazi...Afil 1:20mwa ichi Mulungu sachita manyazi nao...Aheb 11:16abwino m’Khristu akachitidwe manyazi...1 Pet 3:16ngati Mkhristu asachite manyazi...1 Pet 4:16osachita manyazi kwa iye...1Yoh 2:28

CHITA NTCHITO MWALUSO (excels)ukamuona munthu akuchita ntchito zake mwaluso...Miy 22:29[onaninso: pambana]

CHITA NSANJE (envious)pakuti ndinkachita nsanje ...Mas 73:3usamachitira nsanje anthu ochimwa...Miy 24:1makolo athuwo anachita nsanje...Mac 7:9

CHITA CHILENDO (enstranged)oipa achita chilendo...Mas 58:3popeza onsewa asanduka alendo ...Ezek 14:5

CHITA MLANDU (execute)mphamvu yakuchita mlandu...Yoh 5:27[onaninso: langa]

CHITA (accomplished)Yehova anachita...1 Sam 11:13[onaninso: chitidwa, kwanira, kwaniritsidwa]

CHITA (commit)usachite chigololo...Eks 20:14tisachite dama ...1Akor 10:8yense wakuchita tchimo... Yoh 8:34achitanso kusaweruzika...1Yoh 3:4anthu anga anachita...Yer 2:13ndipo anazichita zoyenera...Luk 12:48amene sanachita tchimo...1 Pet 2:22[onaninso: pereka]

CHITA (do)ayambe kuchita zoipa...Mlal 8:11ndafuna kuchita ndi dzachitadi...Yes 46:11akuchitireni, inuyo muwachitire ...Mat 7:12kachiteni zimenezi ndipo...Luk 10:28zimene ndikuona Atate anga akuchita...Yoh 5:19popanda ine, simungathe kuchita kanthu...Yoh 15:5ndichite chiyani kuti ndipulumuke...Mac 16:30tizichita zoipa kuti zabwino...Aro 3:8sindichita zimene ndifuna kuchita...Aro 7:15sindichita zabwino zimene ndifuna...Aro 7:19muzichita zonse kuti...1 Akor 10:31ndingathe kuchita zonse...Afil 4:13chilichonse chimene mungachite...Akol 3:17musanyozere kumachita zachifundo...Aheb 13:16tidzachita chakutichakuti...Yak 4:15

CHITA (exercise)amachita ufumu pa iwo...Mat 20:25[onaninso: chizolowezi cha thupi]

CHITA (made)kuti ndinachita ichi kale...Yes 37:26[onaninso: lenga, panga]

CHITA (work)chochita iwo akupatuka...Mas 101:3zochita zonse ndi zobisika...Mlal 12:14pakuti Ambuye adzachita mau...Aro 9:28[onaninso: chitira, ntchito]

CHITA (worked)zimene Mulungu anachita nao pa...Mac 15:12

Page 31: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: ntchito]

CHITA CHOIPA (hurt)amene apangana kuti andichite choipa...Mas 35:4[onaninso: chitidwa choipa, phwetekwa, pweteka,

pwetekedwa]

CHITA MALIRO (bemoan)musamlire wakufa, musachite maliro ake...Yer 22:10[onaninso:chitira chisoni, lirira, lira]

CHITA UFUMU (dominion)zisachite ufumu pa ine...Mas 19:13uchimo sudzachita ufumu pa inu...Aro 6:14si kuti tichita ufumu pa chikhulupiriro...2 Akor 1:24[onaninso: ulamuliro]

CHITA UFUMU (reigns)Yehova achita ufumu...Mas 93:1[onaninso: lamula]

CHITHATHA (coffin)mfumu Davide anatsata chithatha...2 Sam 3:31nakhudza chithatha...Luk 7:14[onaninso: mtembo]

CHITIDWA (fulfilled)kufikira zitachitidwa zonse...Mat 5:18[onaninso: kwanira, kwaniritsa, kwaniritsidwa]

CHITIDWA (fulfilment)chifukwa zidzachitidwa zinthu zimene...Luk 1:45[onaninso: kwanitsa]

CHITIDWA (accomplished)moyo chitachitidwa...Miy 13:19[onaninso: chita, kwanira, kwaniritsidwa]

CHITIDWA CHOIPA (hurt)sadzachitidwa choipa ndi imfa...Chiv 2:11[onaninso: chita choipa, phwetekwa, pweteka, pwetekedwa]

CHITIRA CHISONI (bemoan)ndani adzakuchitira iwe chisoni...Yer 15:5inu nonse akumzungulira mumchitire iye chisoni...Yer 48:17[onaninso: lirira, lira, chita maliro]

CHITIRA UMBONI (testifies)iyeyu akuchitira umboni...Yoh 3:32Mzimu Woyera andichitira umboni m’midzi yonse...Mac

20:23

CHITIRA CHIFUNDO (courteous)a mtima umodzi, ochitirana chifundo...1 Pet 3:8

CHITIRA ULEMU (glorify)sanamchitira ulemu wakuyenera...Aro 1:21[onaninso: kometsa, lemekeza]

CHITIRA UMBONI (testified)ndipo Yehova anachitira umboni Israele...2 Maf 17:13ndiye akuzichitira umboni...Yoh 19:35monga wandichitira umboni...Mac 23:11pakuchitiratu umboni wa masautso a Khristu...1 Pet 1:11koma umboni wa Mulungu...1 Yoh 5:9

CHITIRA UMBONI (testify)milomo yako ikuchitira umboni wakukutsutsa...Yob 15:6chitani umboni wonditsutsa...Mika 59:12ndipo tichita umboni za chimene tachiona...Yoh 3:11ndipo akundichitira ine umboni ndi iwo omwewo...Yoh 5:39

ndipo tichita umboni kuti Atate anatuma Mwana...1Yoh 4:14

ndatuma mngelo wanga kukuchitirani umboni za...Chiv 22:16[onaninso: neneza]

CHITIRA (work)zithandizana kuwachitira ubwino...Aro 8:28[onaninso: chita, ntchito]

CHITITSA MANTHA (terrify)chisandichititse mantha...Yob 9:34[onaninso: opsa]

CHITITSA MANYAZI (humiliation)kuti atichititse manyazi...Ezara 9:7[onaninso: peputsa, tsitsa]

CHITOLIRO (flute)oyimba zeze ndi chitoliro...Gen 4:21mau a lipenga, chitoliro...Dan 3:5zoyimbira za zingwe ndi chitoliro...Mas 150:4

CHITONTHOZO (consolation)analikulindira matonthozedwe...Luk 2:25chitonthozo chathu chachuluka...2 Akor 1:5muli chitonthozo mwa Khristu...Afil 2:1[onaninso: chisangalatso]

CHITONZO (insults)musaope chitonzo cha anthu...Yes 51:7

CHITSAMBA (bush)mkati mwa chitsamba ...Eks 3:2anakhala mchitsambayo...Deut 33:16womuonekera pachitsamba...Mac 7:35

CHITSANZO (example)ndakupatsani inu chitsanzo...Yoh 13:15amene amatsatira chitsanzo...Afil 3:17tikhale kwa inu chitsanzo...2 Ates 3:9komatu khala chitsanzo...1Tim 4:12nakusiyirani chitsanzo kuti...1 Pet 2:21ataika chitsanzo cha kwa...2 Pet 2:6iikidwa chitsanzo...Yuda 7munayamba kukhala inu chitsanzo...1Ates 1:7

CHITSEKO (door)monga chitseko chimatembenuka...Miy 26:14[onaninso: khomo]

CHITSEKO (gate)chitseko chilichonse chinali cha mwala umodzi...Chiv 21:21[onaninso: khomo, chipata]

CHITSILIZIRO (destiny)sunakumbukira chitsiliziro chako...Mali 1:9

CHITSIME (cistern) ndi kumwa yense madzi a m’chitsime...2 Maf 18:31imwa madzi a m’chitsime mwako...Miy 5:15

CHITSIME (well)njinga yotungira madzi isanathyoke ku chitsime...Mlal 12:6ndipo pamenepo panali chitsime cha Yakobo...Yoh 4:6[onaninso: bwino, koma, komera, limba, ngwiro, pulumutsa]

CHITSIMIKIZO (decree)ndidzauza za chitsimikizo...Mas 2:7[onaninso: chilamulo, lamulo]

CHITSIRIZIRO (end)kufikira chitsiriziro...Aheb 3:6

Page 32: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mwaona chitsiriziro cha Ambuye ...Yak 5:11chitsiriziro cha iwo osamvera...1 Pet 4:17[onaninso: chimaliziro, itha, maliza, mathero, matsiriziro,

tsiriza]

CHITSIRU (fool)kwa chitsiru kulakwa...Miy 10:23chitsiru chidzasanduka kapolo...Miy 11:29wonena mnzake kuti chitsiru...Mat 5:22[onaninso: wopusa]

CHITSOTSO (speck)umaoneranji ka chitsotso...Mat 7:3

CHITSULO (iron)chitsulo chimachiyesa phesi...Yob 41:27chitsulo amachinola nchitsulo...Miy 27:17liri mtsempha wachitsulo...Yes 48:4miyendo yake ya chitsulo...Dan 2:33

CHITSUTSANO (complaint)pakuti Yehova ali nacho chitsutsano...Mika 6:2[naninso: chifukwa, kudandaula]

CHITSUTSO (condemnation)utumiki wa chitsutso unali ndi...2 Akor 3:9pokhala nacho chitsutso...1 Tim 5:12kulandira chitsutso ichi...Yuda 4[onaninso: chilango, chiweruzo]

CHIVOMEREZO (confession)chivomerezo chabwino pamaso pa...1 Tim 6:12amene anachitira umboni chivomerezo...1 Tim 6:13mkulu wansembe wachivomerezo chathu...Aheb 3:1tigwiritsitse chivomerezo chathu...Aheb 4:14[onaninso: lemekeza]

CHIVOMEZI (earthquake)mphepoyo, padachita chivomezi...1 Maf 19:11nthawi ija ya chivomezi...Zek 14:5kudachitika chivomezi chachikulu...Mat 28:2padachitika chivomezi champhamvu...Chiv 6:12

CHIVUNDI (corruption)Mulungu anamuukitsa sananona chivundi...Mac 13:37ku ukapolo wachivundi...Aro8:21lifesedwa muchivundi...1 Akor 15:42kapena chivundi sichilowa...1 Akor 15:50mutapulumuka ku chivundi chiri...2 Pet 1:4adzatuta chivundi...Agal 6:8[onaninso: vunda]

CHIVUTO (distress)chifukwa cha chivuto cha...1 Akor 7:26[onaninso: chisauko, mavuto, nsauko, nsautso, opsa, psinjika,

saukira, sautsika]

CHIWALO (member)chiwalo chako chimodzi...Mat 5:29chiwalo chirichonse cha...Aro 6:13thupitu si chiwalo chimodzi...1 Akor 12:14ndi kachiwalo kakang’ono...Yak 3:5

CHIWEMBU (plot)bwanji anthu akunja akufuna kuchita chiwembu...Mas 2:1adamuuzako za chiwembucho...Mac 9:24

CHIWERENGERO (number)kuti ndidziwe chiwerengero...2 Sam 24:2amadziwa chiwerengero cha nyenyezi...Mas 147:4awerenge chiwerengero cha...Chiv 13:18[onaninso: werenga]

CHIWERUZO (condemnation)koma chiweruzo ndi ichi...Yoh 3:19kukuuka kwa kuweruza...Yoh 5:29[onaninso: chilango, chitsutso]

CHIWOMBANKHANGA (eagle)kumwamba ngati chiwombankhanga...Miy 23:5pamwamba penipeni ngati chiwombankhanga...Yer 49:16zinali nayonso nkhope ya chiwombankhanga...Ezek 1:10chidafanana ndi chiwombankhanga...Chiv 4:7mapiko awiri a chiwombankhanga...Chiv 12:14ndi mapiko monga chiwombankhanga...Yes 40:31[onaninso: mphamba, mphungu]

CHIWONONGEKO (calamities)mpaka chionongeko...Mas 57:1

CHIWONONGEKO (calamity)chionongeko chawo...Deut 32:35[onaninso: choipa, tsoka]

CHIWONONGEKO (destruction)chiwonongeko chikadzafika...Yob 5:21kuchiwonongeko kusowa...Yob 26:6chimgwere modzidzimutsa chiwonongeko...Mas 35:8kapena chiwonongeko chakuthera usana ...Mas 91:6kunyada kumafikitsa kuchiwonongeko...Miy 16:18chiwonongekocho chisanafike...Miy 18:12mudzi wachiwonongeko...Yes 19:18chiwonongeko chituluka...Yer 46:20zokonzekera chiwonongeko...Aro 9:22chiwonengeko chobukapo chidzawagwera...1Ates 5:3amene adzamva chilango ndicho chiwonongeko...2 Ates 1:9zimiza anthu m’chiwonongeko...1Tim 6:9[onaninso: khala fumbi, ononga, onongeka, pasula]

CHIYAMBI (beginning)pachiyambi Mulungu analenga...Gen 1:1ndipo chinkana chiyambi chako...Yob 8:7kumuopa Yehova ndiko chiyambi cha...Mas 111:10Mulungu wazipanga chiyambire...Mlal 3:11Iye amene adalenga athu pachiyambi...Mat 19:4pachiyambi panali mau...Yoh 1:1Chiyambi ichi cha zizindikiro zake...Yoh 2:11anali wambanda kuchokekera pachiyambi...Yoh 8:44muli ndi ine kuyambira chiyambi...Yoh 15:27alibe chiyambi cha masiku ake...Aheb 7:3[onaninso: woyamba]

CHIYAMIKO (thanksgiving)apereke nsembe za chiyamiko...Mas 107:22pamodzi ndi chiyamiko, zopempha...Afil 4:6[onaninso: thokoza]

CHIYANJANO (communion)chiyanjano cha mwazi wa Khristu...1 Akor 10:16kuwala kuyanjana bwanji ndi mdima...2 Akor 6:14chiyanjano cha mzimu woyera...2 Akor 13:14

CHIYANJANO (fellowship)cha atumwi ndi m’chiyanjano...Mac 2:42ku chiyanjano cha mwana wake...1 Akor 1:9inu muyanjana ndi ziwanda...1 Akor 10:20kuunika kuyanjana bwanji...2 Akor 6:14dzanja lamanja la chiyanjano...Agal 2:9musayanjane nazo ntchito za...Aef 5:11chiyanjano chanu chakuthandizira...Afil 1:5ngati chiyanjano cha Mzimu ...Afil 2:1ndi chiyanjano cha zowawa zake...Afil 3:10kuti inunso muyanjane pamodzi...1 Yoh 1:3tikati kuti tiyanjana ndi iye...1Yoh 1:6

Page 33: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

tiyanjana wina ndi mnzake...1 Yoh 1:7

CHIYEMBEKEZO (expectation)kapena chiyembekezo cha...Mas 9:18pakuti chiyembekezo changa...Mas 62:5chiyembekezo cha anthu...Luk 3:15[onaninso: kulindira]

CHIYEMBEKEZO (hope)ndikati, ndiri nacho chiyembekezo...Rut 1:12apitirira opanda chiyembekezo...Yob 7:6ndipo muononga chiyembekezo...Yob 14:19chiri kuti chiyembekezo changa...Yob 17:15nachizula chiyembekezo changa...Yob 19:10chiyembekezo changa chiri...Mas 39:7ndipo chiyembekezo chako...Miy 23:18amoyo onse ali nacho chiyembekezo...Mlal 9:4inu, chiyembekezo cha Israeli...Yer 14:8chikhale khomo la chiyembekezo...Hos 2:15andende a chiyembekezo inu...Zek 9:12ndi kukhala nacho chiyembekezo...Mac 24:15tikondwera mchiyembekezo...Aro 5:2chiyembekezo sichichititsa...Aro 5:5tinapulumutsidwa ndi chiyembekezo...Aro 8:24chiyembekezo chimene sichioneka...Aro 8:24chikhulupiriro, chiyembekezo...1 Akor 13:13chiyembekezo cha kuitana kwake...Aef 1:18akuitanani mchiyembekezo...Aef 4:4chiyembekezo chosungikira kwa...Akol 1:5chiyembekezo cha ulemerero...Akol 1:27chiyembekezo chathu kapena...1Ates 2:19amene alibe chiyembekezo...1 Ates 4:13chisoti chiri chiyembekezo...1 Ates. 5:8Yesu, chiyembekezo chathu...1Tim 1:1m’chiyembekezo cha moyo wosatha...Tit 1:2akulindira chiyembekezo...Tit 2:13kuchigwira chiyembekezo...Aheb 6:18kulowa nacho chiyembekezo...Aheb 7:19anatibalanso ku chiyembekezo...1 Pet 1:3chifukwa cha chiyembekezo...1 Pet 3:15wakukhala nacho chiyembekezo...1Yoh 3:3[onaninso: yembekeza]

CHIYERETSO (holiness)sanatiitana ife titsate chidetso koma chiyeretso...1 Ates 4:7[onaninso: chiyero, patulika, woyera]

CHIYERO (holiness)Mulungu walankhula m’chiyero...Mas 60:6ndinalumbira kamodzi m’chiyero...Mas 89:35chiyero chiyenera nyumba...Mas 93:5monga mwa Mzimu wa chiyero...Aro 1:4ndi kutsiriza chiyero m’kuopa...2 Akor 7:1kuti tikalandire nao pa chiyero chake...Aheb 12:10[onaninso: chiyeretso, patulika, woyera]

CHIZINDIKIRITSO (understanding)mukadzazidwe ndi chizindikiritso...Akol 1:9[onaninso: chidziwitso, kumvera, kuzindikira, luntha, luso,mvetsa, nzeru]

CHIZINDIKIRO (mark)ndipo Yehova anaika chizindikiro...Gen 4:15alembedwe chizindikiro pa dzanja...Chiv 13:16amene analembedwa chizindikiro...Chiv 14:11[onaninso: ona]

CHIZOLOWEZI CHATHUPI (exercise)uzizoloweretse kuchita chilungamo...1 Tim 4:7chizolowezi cha thupi chipindula...1 Tim 4:8[onaninso: chita, yesa]

CHOFUNDA (mantle)

ndipo anatenga chofunda cha...2 Maf 2:14

CHOFUNDA (wing)ndinakufuna chofunda changa...Ezek 16:8[onaninso: phiko]

CHOFUNIKA (pleasant)chakudya chofunika osachidya ine...Dan 10:3[onaninso: bwino, koma, kometsera, kondwera, kondweretsa]

CHOIPA (calamity)kodi choipa chidzagwera mudzi...Amo 3:6[onaninso: chiwonongeko, tsoka]

CHOIPA (disaster) sudzaopanso choipa...Zef 3:15 [onaninso: kuonongeka, tsoka]

CHOIPA (evil)palibe choipa chidzakukhudza...Yob 5:19chokoma chinadza choipa...Yob 30:26wakukondwera nacho choipa...Mas 5:4sindidzaopa choipa chirichonse...Mas 23:4choipa chitsata mwini...Mas 34:21ukonda choipa kuposa chabwino...Mas 52:3palibe choipa chidzakugwera...Mas 91:10pali choipa chovuta ...Mlal 5:13ichi ndi choipa m’zonse...Mlal 9:3achotsedwa pa choipa...Yes 57:1a mtendere, si a choipa ayi...Yer 29:11muchitira miyoyo yanu choipa...Yer 44:7chokoma, si choipa ayi...Amo 5:14atulutsa zoipa m’chuma chake choipa...Mat 12:35chitchule choipacho...Yoh 18:23koma choipa chimene ine sindifuna...Aro 7:19pamene ndifuna chabwino, choipa chiriko...Aro 7:21chirichonse chabwino kapena choipa...Aro 9:11musabwezere choipa okondedwa...Aro 12:9musabwezere choipa...Aro 12:17musagonjere kwa choipa koma...Aro 12:21ndi chabwino gonjetsani choipa...Aro 12:21maonekedwe onse a choipa...1Ates 5:22[onaninso: oipa, woipa, zoipa]

CHOIPA (wickedness)ndichite chinthu choipitsitsa...Gen 39:9Mulungu sangachite choipa...Yob 34:12sindidzalola choipa...Mas 101:4[onaninso: ipa, zoipa]

CHOKA (depart)ndodo yachifumu siidzachoka...Gen 49:10adati kwa Mulungu, tichokereni...Yob 21:14mapiri adzachoka...Yes 54:10chokani kwa ine otembereredwa...Mat. 25:41nditachoka ine, adzalowa...Mac 20:29[onani: futuka, patuka]

CHOKA (disappears)madzi achoka m’nyanja...Yob 14:11

CHOKHUMUDWITSA (offense)ndiwe chokhumudwitsa...Mat 16:23[onaninso: chikhumudwitso, khumudwa,khumudwitsa, lakwa,lakwitsa]

CHOLAKWA (fault)koma sadapeze cholakwa...Dan 6:4mukhale angwiro ndi osalakwa...Afil 2:15alibe cholakwa...Chiv 14:5[onaninso: chifukwa]

CHOLANGA (plague)ndipo cholanga sichidzayandikiza hema...Mas 91:10

Page 34: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: mliri]

CHOLEMETSA (weight)titaye cholemetsa chilichonse...Aheb 12:1[onaninso: kulemera, miyeso, muyeso]

CHOLENGEDWA (creation)cholengedwacho cha gonjetsedwa...Aro 8:20[onaninso: chilengedwe, wolengedwa]

CHOLENGEDWA (creature)cholengedwa chonse cha Mulungu...1 Tim 4:4palibe cholengedwa chosaonekera...Aheb 4:13ndipo cholengedwa chilichonse...Chiv 5:13[onaninso: olengedwa, zamoyo]

CHOLOWA (heritage)mwandipatsa cholowa...Mas 61:5ichi ndi cholowa cha atumiki...Yes 54:17ndi cholowa changa Israeli...Yow 3:2nkhosa za cholowa chanu...Mika 7:14[onaninso: gawo, lanulanu]

CHOMBO (ark)udzimangire chombo...Gen. 6:14[onaninso:chingalawa, likasa la pangano]

CHOONA (truth)ndine choona ndiponso...Yoh 14:6choona nchiyaninso...Yoh 18:38kuyera mtima ndi wa choona...1 Akor 5:8mutavala ndi choona...Aef 6:14chokana kukonda choona...2 Ates 2:10ndi kuzindira choona...2 Tim 2:25sangathe kudziwa konse choona...2 Tim 3:7wonse choona chimene...2 Pet 1:12njira ya choona...2 Pet 2:2kuti tili ndi choona...1 Yoh 3:19pakuti Mzimuyo ndiye choona...1 Yoh 5:6moyo wake m’choona...3 Yoh 3[onaninso: choonadi, lungama, zoona]

CHOONADI (truth)chifundo chanu ndi choonadi chanu zindisunge...Mas 40:11choonadi chiphukira mdziko...Mas 85:11choonadi chake ndicho chikopa chotchinjiriza...Mas 91:4musandichotsere ndithu mau a choonadi...Mas 119:43chiwerengero cha mau anu ndicho choonadi...Mas 119:160koma si pa choonadi pakuti alinkunkabe nachita zoipa...Yer 9:3popeza palibe choonadi kapena chifundo...Hos 4:1Yerusalemu adzatchedwa mudzi wa choonadi...Zek 8:3nenani choonadi yense ndi mnzake...Zek 8:16mudachimva kale m’mau a choonadi cha...Akol 1:5[onaninso: choona, lungama, zoona]

CHOOPSA (horrible)chodabwitsa ndi choopsa...Yer 5:30ndinaona chinthu choopsetsa...Hos 6:10

CHOOPSA (terror)muona choopsa muchitapo mantha...Yob 6:21sudzaopa choopsa chausiku...Mas 91:5ndidzakuyesa iwe choopsa...Yer 20:4[onaninso: kunjenjemera, mantha, opsa]

CHOPEREKA (offering)akabwera nacho chopereka...Lev 1:2nsembe ndi chopereka simukondwera...Mas 40:6nsembe ndi chopereka simunazifuna...Aheb 10:5cha machimo palibenso chopereka cha kwa uchimo...Aheb

10:18[onaninso: nsembe, zopereka]

CHOPONDAPO MAPAZI (footstool)kukhala ngati chopondapo mapazi...Mas 110:1akhale ngati chopondapo mapazi...Mat 22:44onaninso: mpando wa mapazi]

CHOPOSA (exceeding)zirinkudza chuma choposa...Aef 2:7

CHOTSA (blow)yopweteka ichotsa zoipa...Miy 20:30[onaninso: omba]

CHOTUPITSA (leaven)tsiku loyamba mudzichotsa chotupitsa...Eks 12:15uli wofanana ndi chotupitsa mikate...Mat 13:33yang’anirani mupewe chotupitsa mkate...Mat 16:6chotupitsa pang’ono chitupitsa mtanda...1 Akor 5:6chotupitsa pang’ono chitupitsa mtanda...Agal 5:9

CHOVALA (apparel)mchovala chake...Yes 63:1onse akuvala chovala...Zef 1:8aziveke okha ndi chovala...1Tim 2:9ndi chovala chokometsetsa...Yak 2:2kapena kuvala chovala...1 Pet 3:3

CHOVALA (garment)chovala chodyedwa ndi numbi...Yob 13:28chovala changa ndinayesa chiguduli...Mas 69:11kuunika monga ndi chovala...Mas 104:2munthu wosavala chovala...Mat 22:11

CHOVALA (garments)ana ankhosa adzakupatsa chovala...Miy 27:26zimakhala ngati chovala chake...Miy 31:25ndi thupi loposa chovala...Mat 6:25ndi chovala choyera...Mat 28:3[onaninso: zovala]

CHOWA (beard)ndinagwira chowa lake...1 Sam 17:35[onaninso: ndevu]

CHOWIRINGULA (excuse)tsopano palibe chowiringula...Yoh 15:22[onaninso: phophonya, wiringula]

CHOZIZWITSA (miracle)‘chitani chozizwitsa kuti...Eks 7:9adachitadi chizindikiro chozizwitsa...Mac 4:16[onaninso: champhamvu]

CHOZOKOTERA (pen)ndi chozokotera chachitsulo ndi kuthira mtovu...Yob 19:24[onaninso: peni]

CHULUKA (abound)chifukwa cha kuchuluka kwa...Mat 24:12pamene uchimo unachuluka...Aro 5:20kuti chisomo chichuluke...Aro 6:1chuchulukitsire chiyamiko...2 Akor 4:15kuchulukitsa chisomo...2 Akor 9:8chulukani koposa...1 Ates 4:1ndipo zikachuluka...2 Pet 1:8kulakwa kukachuluke...Aro 5:20ndi wa chifundo chochuluka...Mas 103:8akuchuluka muntchito...1 Akor 15:58

CHULUKA (abundance)uli nawonso antchito ochuluka ofukula miyala...1 Mbir 22:15

Page 35: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi mtendere wochuluka kufikira sipadzakhala...Mas 72:7pakuti anaponyamo onse mwa zochuluka zao...Marko 12:44sulingana ndi kuchuluka kwa zinthu zake ali nazo...Luk 12:15kusauka kwao kwenikweni zidachulukira ku cholemera...2

Akor8:2[onaninso: chuma, mphamvu, ukulu, sefukira, yambiri, zonona]

CHULUKA (abundant)ndi wochuluka chifundo ndi choonadi...Mas 86:15m’zivutitso mochulukira, mndende mochulukira...2 Akor 11:23koma chisomo cha Ambuye wathu chidachulukatu pamodzi...1Tim 1:14[onaninso: dzala, kulu]

CHULUKA (abundantly)ndi kukhala nawo wochuluka...Yoh 10:10Mulungu pofuna kuonetsera mochulukira kwa...Aheb 6:17[onaninso: posa, zonona]

CHULUKA (manifold)ntchito zanu zichulukadi...Mas 104:24[onaninso: mitundu mitundu]

CHULUKITSA (multiplied)amadzichulukitsira mavuto...Mas 16:4ophunzira ankachulukirachulukira...Mac 6:7koma mau a Mulungu anakula nachulukitsa...Mac 12:24

CHULUKITSA (multiply)zibalane, zichuluke...Gen 1:22ndidzachulukitsa ndithu mbeu...Gen 16:10ndidzachulukitsa masiku...Yob 29:18chomwecho ndidzachulukitsa...Yer 33:22

CHUMA (abundance)ngakhale wokonda chuma sadzakhuta phindu...Mlal 5:10aturutsa zabwino mchuma chake chabwino...Mat 12:34[onaninso: chuluka, mphamvu, ukulu, sefukira,yambiri,

zonona]

CHUMA (goods)uli nacho chuma chambiri chosungika...Luk 12:19ali kumwaza chuma chake...Luk 16:1koma iye amene ali nacho chuma cha...1 Yoh 3:17[onaninso: katundu, zanga, zinthu]

CHUMA (riches)chuma ndi ulemu zimachokera...1 Mbir 29:12amapeza chuma, koma...Yob 20:15munthu amakundika chuma...Mas 39:6koma adakhulupirira chuma...Mas 52:7chuma chikachuluka...Mas 112:3imene imakuninkha chuma...Miy 3:16ndili nacho chuma...Miy 8:18chuma sichithandiza konse...Miy 11:4wokhulupirira chuma chake...Miy 11:28m’menemo ali nchuma chochuluka...Miy 13:7nyumba ndi chuma...Miy 19:14woopa Chauta ndi chuma...Miy 22:4chuma sichikhala mpaka...Miy 27:24chuma chopweteka mwini wake...Mlal 5:13ndidzakupatsa chuma...Yes 45:3mudzadyerera chuma...Yer 61:6munthu wopeza chuma...Yer 17:11udachulukitsa chuma chako...Ezek 28:5kwa anthu achuma...Marko 10:23chuma chopanda malire...Aef 3:8kapena kudalira chuma...1Tim 6:17kunali chuma chachikulu...Aheb 11:26chuma chanu chaola...Yak 5:2kulandira mphamvu, chuma...Chiv 5:12

CHUMA (treasure)Yehova adzakutsekulirani chuma chake chokoma...Deut 28:12amene wapeza chuma...Mas 119:162Israeli kuti akhale chuma...Mas 135:4amakhala ndi chuma chambiri...Miy 15:6ndiko kumapezesa chuma...Yes 33:6kumene kuli chuma...Mat 6:21zabwino m’chuma chabwino...Mat 12:35m’nkhokwe ya chuma...Mat 13:52chuma udzachipeza kumwamba...Mat 19:21amene amadziwunjikira chuma...Luk 12:21chabe zosungiramo chuma...2 Akor 4:7mwazikundikira chuma masiku otsiriza...Yak 5:3

CHUMA (treasures)amaifunafuna kupambana chuma...Yob 3:21kumaiwunguza ngati chuma...Miy 2:4chuma chochipeza monyenga...Miy 21:6chuma chao nchosatha...Yes 45:3kuiwala chuma chimene...Mika 6:10musadziwunjikire chuma...Mat 6:19iyeyu adzapeza chuma...Akol 2:3kunali chuma chachikulu...Aheb 11:26

CHUMA (wealth)“ndapeza chuma chonsechi...Deut 8:17wake wachuma kwambiri...Rut 2:1sudapemphe katundu, chuma...2 Mbir 1:11amangokhulupirira chuma chao...Mas. 49:6chuma cha munthu wolemera...Miy 10:15chuma chochipeza mofulumira...Miy 13:11chuma chimachulukitsa abwenzi...Miy 19:4adzabwera ndi chuma chao...Yes 60:11

CHUMBA (barren)ine chumba chabala asanu ndi awiri...1 Sam 2:5kondwera, chumba iwe osabala...Agal 4:27[onaninso: kusabala, opanda zipatso, uma, wosaonamwana]

CHURUKA (length)ndi masiku anu ochuruka...Deut 30:20[onaninso: litali]

DDABWA (amazed)

kunthunthumira ndi kudabwa...Marko 16:8

DABWA (astonished)ndi onse amene anamva iye anadabwa...Luk 2:47[onaninso: zizwa]

DABWA (marvel)musadabwe nazo zimenezi...Yoh 5:28

DABWA (marveled)kotero kuti Pilato adadabwa...Marko 15:5chirombocho ali odabwa...Chiv 13:3mkaziyo, ndidadabwa kwambiri...Chiv 17:6[onaninso: zizwa]

DABWITSA (astonishment)ndipo mudzakhala chodabwitsa...Deut 28:37kudabwa kwandigwira...Yer 8:21

DABWITSA (wonderful)dzina laketu nlodabwitsa...Ower 13:18chinali chodabwitsa...2 Sam 1:26zinthu zodabwitsa kwa ine...Yob 42:3mboni zanu nzodabwitsa...Mas 119:129

Page 36: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

Phungu wodabwitsa...Yes 9:6uphungu wake ndi wodabwitsa...Yes 28:29adaona zodabwitsa…Mat 21:15[onaninso: zazikulu]

DAGONI (Dagon) mulungu wa Afilisiti...Ower 16:23 anagwa pansi patsogolo palikasa la Yehova...1 Sam 5:1-5

DALA (blessed)zidzakhala zodala...Deut 28:4[onaninso: dalitsa, dalitsidwa, dalitsika, odala, wodala]

DALIMATIYA (Dalmatia)dera kumwera kwa nyanja ya Adriatik, Tito ananyamukakupitako...2 Tim 4:10

DALIRA (lean)usadalire nzeru zako...Miy 3:5[onaninso: tsamira]

DALITSA (bless)ndidzadalitsa iwo akudalitsa iwe...Gen 12:3ukapanda kundidalitsa ine...Gen 32:26Yehova akudalitse iwe...Num 6:24adzadalitsa nyumba ya Israeli...Mas 115:12adzadalitsa iwo akuopa Yehova...Mas 115:13dalitso la Mulungu likhale pa inu...Mas 129:8ndidzadalitsatu chakudya chake...Mas 132:15dalitsani iwo akutemberela inu...Luk 6:28dalitsani iwo akutemberera inu...Aro 12:14polalatiridwa tidalitsa...1Akor 4:12[onaninso: lemekeza, yamika]

DALITSA (blessed)Mulungu ndipo anadalitsa...Gen 1:22wodalitsika aliyense wakudalitsa iwe...Gen 27:29ntchito ya manja ake mwaidalitsa...Yob 1:10[onaninso: dala, dalitsidwa, dalitsika, odala, wodala]

DALITSA (prosper)pakuti Mulungu adamdalitsa...2 Mbir 26:5[onaninso: lemera, lemereza, pindula, phindu]

DALITSIDWA (blessed)wamn’gono adalitsidwa ndi...Aheb 7:7[onaninso: dala, dalitsa, dalitsika, odala, wodala]

DALITSIKA (blessed)adzadalitsika munthu wakuopa...Mas 128:4Inu odalitsika a atate...Mat 25:34[onaninso: dala, dalitsa, dalitsidwa, odala, wodala]

DALITSO (blessing)ndidzauza dalitso langa...Lev 25:21ndili kuika pamaso panu dalitso lero...Deut 11:26dalitso la iye akati...Yob 29:13dalitso lanu likhala pa anthu...Mas 3:8kwa chidalitso kwa Khristu...Aro 15:29mudzakhala chodalitsa...Zek 8:13chikho cha dalitso chimene tidalitsa...1Akor 10:16kuti dalitso la Abraham...Agal 3:14anatidalitsa ife ndi dalitso...Aef 1:3irindira dalitso lochokera kwa Mulungu...Aheb 6:7anafuna kulowa dalitsolo anakanidwa...Aheb12:17

DALITSO (blessings)dalitso ndi tembelero...Yos 8:34[onaninso: madalitso]

DAMA (harlotry)dama lake linaipitsa dziko...Yer 3:9

ndi chinyerinyeri cha dama lako...Yer 13:27

DAMASIKO (Damascus)mzinda waukulu wa Siriya, unatengedwa ndi Davide...2 Mas8:5,6;1 Maf 11:23,24;15:18Elisa ananeneramo...2 Maf 8:7-15unaneneredwa uneneli...Yes 8:3,4unatengedwa ndi Asuri ...2 Maf 16:9Paulo anasinthika panjira yopita kumeneko,Paulo analalikirako koyambirira ...Mac 9:1-22anathawako Paulo...2 Akor 11:32,33anapitakonso...Agal 1:17

DANA (abhor)muzidana ndi zoipa...Aro 12:9[onaninso: ipidwa, nyansa, nyansidwa]

DANDAULA (complain)munthu wamoyo adandauliranji...Mali 3:39munadandaula M’mahema...Deut 1:27koma adandaula M’mahema...Mas 106:25monga ena aiwo adadandaula...1 Akor 10:10

DANDAULA (pray)ndidzadandaula ndi kubuula...Mas 55:17[onaninso: pempha, pemphera, pempherera]

DANDAULIRA (beg)okondedwa ndikukudandaulirani...1 Pet 2:11[onaninso: pembedza, pempha]

DANDAULIRA (exhort)tiwalamurile ndi kuwadandaulira...2 Ates. 3:12udandaurile ngati tate...1Tim 5:1dandaulirani nokha tsiku ndi tsiku...Aheb 3:13[onaninso: chenjeza]

DANI (Dan)mwana wamwamuna wa Yakobo wobelekedwa ndiBilaha...Gen 30:5,6ananeneredwa uneneri...Gen 49:16,17— fuko :linawerengedwa...Num 1:38,39lodalitsidwa...Deut 33:22analandira cholowa...Yos 19:40-47anagwa mukupembedza mafano...Ower 18:1-31— mzinda, malire a kumpoto kwa Israeli...Ower 20:1wotchedwa Lesemu ; wogonjetsedwa ndi ana a Dani...Yos

19:47malo akulu opembedzera mafano...1 Maf 12:28-30anaonongedwa ndi Beni-hadadi...1 Maf 15:20

DANIELI (Daniel)anatengedwa kupita ku Babulo; anakana chakudya chaNebukadineza...Dan 1anamasulira maloto, analemekezedwa ndi mfumu...Dan 2anamasulira zolembedwa pakhoma,analemekezedwa ndi Belisazara...Dan 5:10-29anakwezedwa pantchito; anachitilidwa chiwembu,naponyedwa m’dzenje la mikango...Dan 6:1-23anaona masophenya azamoyo zinai, nkhosa ya mphongo nditonde...Dan 7;8anapembedzera Israeli...Dan 9:1-19anaona masompenya ena...Dan 9:20;12:13

DARIYO (Darius)Daliyo mwana wa Ahaswero, wa mbeu ya Amedi,anakhala mfumu ya Akasadi...Dan 9:1analowa ufumu pamalo a ufumu wa Berisazala...Dan 5:30,31analamulira limodzi ndi Koresi...Dan 6:28— Daliyo Hasitapisi (522-486B.C), mfumu ya Perisiya yense,

Page 37: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ntchito yomanga kachisi inagwiridwa pansi paulamuliro wake...Ezara 4:5,24anatsimikiza chikalata cha ulamuliro wa mfumu Koresi ...Ezara6:1-14— Dariyo wa ku Perisiya (423-404) B.C.zolembedwa za unsembe zinasungidwa nthawi ya ulamulirowake...Neh 12:22

DATANI (Dathan)analowa nao mukuukira kwa Kora...Num 16:1-35anamezedwa ndi nthaka...Mas 106:17

DAVIDE (David)anadzodzedwa ndi Samueli...1 Sam 16:1-13anakhala oyimba zeze kwa mfumu...1 Sam 16:14-23anagonjetsa Goliati...1 Sam 17anapanga pangano ndi Yonatani...1 Sam. 18:1-4analemekezedwa ndi Saulo; anakondedwa ndi anthu,Saulo anayamba kumchitira nsanje...1 Sam 18:5-16anapatsidwa Mikala kukhala mkazi wake...1 Sam 18:17-30anamthawa Saulo...1 Sam 19:20;21:10—22:5;23:14-29anadya mkate wopatulika...1 Sam 21:1-6;Mat 12:3,4anapulumutsa Keila kuchokera kwa Afilisti...1 Sam 23:1-13kawiri konse anasunga moyo wa Saulo...1 Sam 24:1-22;26:1-25mkwiyo wake pa Nabala unakondweretsedwa ndi Abigayeli;anamkwatira iye...1 Sam 25:2-42anapanga mgwirizano ndi Afilisti...1 Sam 27:1-28:2anakanidwa ndi iwo...1 Sam 29anabwezera kuonongeka kwa Zikilaga...1 Sam 30analira pa maliro a Saulo ndi Yonatani...2 Sam 1anadzodzedwa kukhala mfumu ya Yuda...2 Sam 2:1-7anamenya nkhondo ndi a m’nyumba ya Saulo;Abineri anamsiya Davide...2 Sam 3:1,6-21analira maliro a Abineri...2 Sam 3:28-39analanga anthu amene ananyonga Isiboseti...2 Sam 4adzodzedwa kukhala mfumu ya Israeli yense...2 Sam 5:1-5anagonjetsa Yerusalemu, anasandutsa Yerusalemu mzindawaukuru waIsraeli...2 Sam. 5:6-16anagonjetsa Afilisti...2 Sam 5:17-25anabweretsanso likasa la Mulungu ku Yerusalemu...2 Sam 6analandira pangano losatha...2 Sam 7anagonjetsabe...2 Sam 8,10anamchitira chifundo Mefiboseti...2 Sam 9anachita tchimo la chigololo ndi kupha...2 Sam 11anadzudzulidwa ndi Natani; analapa...2 Sam 12:1-23;Mas 32;51anaukiridwa ndi Abisalomu...2 Sam 15-18analira maliro a Abisalomu...2 Sam 18:33-19:8anadzionetsera wa chifundo...2 Sam 19:18-39kuukira kwa Seba...2 Sam 19:40-20:22anabwezera kwa Agibeoni...2 Sam 21:1-14anayimba nyimbo ya chiombolo...2 Sam 22anachimwa powerenga anthu...2 Sam 24:1-17anatanganitsidwa kukonza malo oti amangirepo guwa laYehova...2 Sam 24:18-25anasunga malo a ufumu a Solomoni...1 Maf 1:5-53anapereka malangizo kwa Solomoni...1 Maf 2:1-11mau ake omaliza...2 Sam 23:1-7anauziridwa ndi mzimu...Mat 22:43monga m’neneri...Mac 2:29-34chikhulupiriro chake...Aheb 11:32-34

DAZI (Baldhead)takwera wadazi...2 Maf 2:23

DEBORA (Deborah)m’neneri wamkazi komanso oweruza...Ower 4:4-14anayimba ndi kupanga nyimbo ya chipambano...Ower 5:1-31

DELAYA (Delaiah)mwana wa Semaya; anapempha mfumu kuti asatenthe mpukutu

wa Yeremiya...Yer 36:12,25

DELILA (Delilah)anamnamiza Samisoni...Ower 16:4-22

DEMA (Demas)anamtsatira Paulo...Akol 4:14anamleka Paulo...2 Tim 4:10

DEMETRIYO (Demetrius)wosula siliva ku Efeso...Mac 19:24-31mkhristu wabwino...3 Yoh 12

DERA NKHAWA (worry)musadere nkhawa moyo wanu...Mat 6:25musamada nkhawa nkumanena...Mat 6:31

DERBE (Derbe)Paulo anapitako...Mac 14:6,20Paulo anakumanako ndi Timoteo...Mac 16:1

DETSEDWA (darkened)odetsedwa nzeru zao...Aef 4:18

DETSEDWA (defiled)pakuti manja anu adetsedwa...Yes 59:3sanalowa ku Pretorio kuti angadetsedwe...Yoh 18:28kwa iwo odetsedwa...Tit 1:15komatu zadetsedwa nzeru zao...Tit 1:15[onaninso: ipitsa]

DETSA (defile)mkulota kwawo adetsa matupi...Yuda 8[onaninso: ipitsa]

DAIMONDI (diamond)cha nsonga ya mwala wa daimondi...Yer 17:1

DIBIRI (Debir)mzinda wa mu Yuda; unatengedwa ndi Yoswa...Yos 10:38,39unatengedwanso ndi Otimeli; unkatchedwa Kiriyati-SeferiYosw 15:15-17;Ower 1:11-13

DIBONI (Dibon)mzinda a Amori...Num 21:30unatengedwa ndi Israeli...Num 32:2-5zachiongeko chake zinanenedweratu...Yer 48:18:22

DIKIRA (awake)ndidikira ndikhala ngati mbawa...Mas 102:7[onaninso: galamuka, khala maso, kumika, uka]

DIKIRA (wait)ndidzadikira mpaka kumasulidwa...Yob 14:14umdikire mosadandaula...Mas 37:7Yehova adzadikira...Yes 30:18amene adikira Yehova...Yes 40:31mkwabwino kudikira Chauta...Mali 3:26amene akudikira Mbuye...Luk 12:36ndi maso, timazidikira mopirira...Aro 8:25mgonero wa Ambuye, muzidikirana...1 Akor 11:33mukudikira mwana wake...1 Ates 1:10[onaninso: yembekeza]

DIKIRA (waited)ankadikira Zakariya...Luk 1:21Mulungu adaadikira moleza...1 Pet 3:20[onaninso: yembekeza]

DIKIRA (waiting)ngwodala amene andimvera nadikira pa zitseko zanga...Miy

8:34

Page 38: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

podikira kuti Mulungu...Aro 8:23kumeneko akudikira...Aheb 10:13[onaninso: kulindira, yembekezera]

DIKIRA (waits)wachigololo amadikira...Yob 24:15[onaninso: yembekeza]

DINA (Dinah)mwana wamkazi wa Leya...Gen 30:20,21anadetsedwa ndi Sekemu...Gen 34:1-24azichimwene ake anabwezera...Gen 34:25-31

DIOTREFE (Diotrephes)membala wovuta wa mpingo...3 Yoh 9,10

DISO (eye)diso kulipa diso...Eks 21:24ndidzakupangira ndi diso...Mas 32: 8diso la Yehova lili paiwo...Mas 33:18iye wakuwumba diso....Mas 94:9ndi diso lopenya...Miy 20:12amene ali ndi diso lachifundo...Miy 22:9mwini diso la nkhwezule...Miy 28:22diso lochitira atete ake...Miy 30:17ngakhale diso silikhuta...Mlal 4:8ngakhale diso silinaona...Yes 64:4akhuza mwana wa diso lake...Zek 2:8diso lako lakumanja likulakwitsa...Mat 5:29diso kulipa diso...Mat 5:38mtandawo ulimo diso lakolo...Mat 7:3ngati diso lako likukhumudwitsa...Mat 18:9diso lako laipa kodi...Mat 20:15ufumu wa Mulungu ndi diso...Marko 9:47ngamira ipyole diso lasingano...Luk 18:25popeza sindiri diso...1 Akor 12:16thupi lonse likadakhala diso...1 Akor 12:17m’kutwanima kwadiso...1Akorinto 15:52diso lililonse lidzapenya...Chiv 1:7[onaninso: maso]

DOEGI (Doeg)Mu-edomu; wamkuru wa anthu woyang’anira ziweto za

Saulo...1Sam 21:7anampereka Davide...1 Sam 22:9,10)anapha ansembe makumi asanu ndi atatu ndi mphambu zisanu(85)...1 Sam 22:18,19

DONGO (clay)kodi dongo linganene...Yes 45:9ife tiri dongo...Yes 64:8mwina chitsulo, mwina dongo...Dan 2:33[onaninso: dothi]

DORIKA (Dorcas)wophunzira wa ku Yopa, wotchedwanso Tabita;anaukitsidwa...Mac 9:36-42

DOTHI (clay)iwo akukhala m’nyumba za dothi...Yob 4:19kuti mwandiumba ngati dothi...Yob 10:9zikunga malinga a dothi...Yob 13:12inenso ndinaumbidwa ndi dothi...Yob 33:6lisandulika ngati dothi...Yob 38:14woumba adayesedwa ngati dothi...Yes 29:16monga dothi dzanja la woumba...Yer 18:6sakutha kuchita zake pa dothi...Aro 9:21[onaninso: dongo]

DOTHI (dust)anaumba munthu ndi dothi lapansi...Gen 2:7

udzabwereranso ku dothi komweko...Gen 3:19uchiwone ngati dothi...Yob 22:24lisamakhaleponso dothi...Miy 8:26zonsezi zinachokera ku dothi...Mlal 3:20ndani adayesa dothi...Yes 40:15adavivinika pa dothi ngati...Mika 7:17munthu wopangidwa ndi dothi...1 Akor 15:49[onaninso: fumbi]

DUDUKIRA (share)mlendo sadudukira ndi chimwemwe chake...Miy 14:10[onaninso: gawana, gawira]

DUKIDWA (proud)wodukidwa mtima aputa makangano...Miy 28:25[onaninso: kudzikuza, kudzitama, nyada]

DULA PAKATI (divide)m’duleni pakati mwana wamoyoyu...1 Maf 3:25[onaninso: gawa, gawikana]

DULA (cut)likulakwitsa iwe, ulidule...Mat 5:30nadzamdula, nadzaika...Mat 24:51amene Petro anamdula khutu...Yoh 18:26[onaninso: dulidwa]

DULA (circumcise)potero dulani khungu...Deut 10:16Yehova Mulungu wanu adzakudulani...Deut. 30:6mudzidulire nokha kwa Yehova...Yer 4:4kuyenera kuwadula iwo...Mac 15:5

DULIDWA MUTU (beheaded)anatumiza mnyamata namdula mutu...Mat 14:10amene anawadula khosi...Chiv 20:4

DULIDWA (circumcised)adzidulidwa amuna onse...Gen 17:10akusadulidwa mwa chikhulupiriro...Aro 4:10ngati mulola akuduleni...Agal 5:2wodulidwa tsiku lachisanu...Afil 3:5amenenso munadulidwa mwa iye...Akol 2:11

DULIDWA (cut)ochita zoipa adzadulidwa...Mas 37:9achiwembu adzadulidwamo...Miy 2:22[onaninso: dula]

DURUSILA (Drusilla)mkazi wa Felikisi, amvetsera kwa Paulo...Mac 24:24,25

DUTSA (pass)pamene ukudutsa pamoto...Yes 43:2[onaninso: pita, pitirira]

DUWA (flower)atuluka ngati duwa...Yob 14:2aphuka monga duwa...Mas 103:15duwa lakufota la ulemerero...Yes 28:4kunga kwa duwa la m’nthengo...Yes 40:6udzu unyala, duwa lifota...Yes 40:7ulemerero wao wonse ngati duwa...1 Pet 1:24[onaninso: unamwali]

DWACHEDWACHE (disorderly)yense wakuyenda dwachedwache osatsata mwambo...2 Ates 3:6[onaninso: chipolowe]

DYANA (devour)ngati mulumana ndi kudyana...Agal 5:15[onaninso: dyera, idya, likwira]

Page 39: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

DYERA (appetite)ngati uli wadyera...Miy 23:2[onaninso: chakudya]

DYERA (devour)amasiye nkumawadyera...Mat 23:14[onaninso: dyana, idya, likwira]

DYETSA (fed)Mulungu amene amadyetsa ine...Gen 48:15nakudyetsani ndi mana...Deut. 8:3abusawo anandidyetsa okha...Ezek 34:8ndinadyetsa inu mkaka...1 Akor 3:2

DYETSA (feed)kuti adzikudyetsa kumeneko ...1 Maf 17:4ya olungama imadyetsa ambiri...Miy 10:21ndikudyetsa magulu ako ...Yes 61:5dyetsa ana a nkhosa anga ...Yoh 21:15dyetsa nkhosa zanga ...Yoh 21:17wakumva njala, umdyetse ...Aro 12:20chuma changa kudyetsa osauka ...1 Akor 13:3

DYETSA (feeds)wa Kumwamba azidyetsa...Mat 6:26[onaninso: kudya]

DZADZA (fill)mudzadze dziko lonse la pansi ...Gen 1:28ndikudzadza nyumba zawo...Miy 8:21Ine sindidzala kumwamba ...Yer 23:24ndipo ndidzadza nyumba iyi ...Hagai 2 :7dzadzani mitsukoyo ...Yoh 2 :7kuti adzadze zithu zonse...Aef 4:10dzadza machimo ao...1 Ates 2:16

DZADZA (filled)ulemerero wake udzadze...Mas 72:19mitima yao idadzadza...Aro 1:29moyo wanu udzakhala wodzadza...Afil 1:11[onaninso: dzadzidwa, dzala, khuta]

DZADZA (full)amene anadzadza nayo phodo...Mas 127:5koma nyanjayo osadzadza...Mlal 1:7ulemerero wake wadzadza dziko...Yes 6:3chigwacho chinali chodzadza ndi mafupa...Ezek 37:1Chauta wandidzadza ndi mphamvu...Mika 3:8[onaninso: dzadzidwa, dzala]

DZADZIDWA (filled)odzadzidwa ndi kudziwitsa konse...Aro 15:14kuti mudzadzidwe kotheratu...Aef 3:19koma mudzadzidwe ndi Mzimu...Aef 5:18[onaninso: dzadza, dzala, khuta]

DZADZIDWA (full)munthu wodzadzidwa ndi chikhulupiriro...Mac 6:5[onaninso: dzadza, dzala]

DZALA (abundant)Inu ndinu Mulungu wachisomo ndi wodzala chifundo...Jona 4:2[onaninso: chuluka, kulu]

DZALA (dunghill)pa munda kapsena pa dzala...Luk 14:35

DZALA (filled)pakamwa pathu panadzala...Mas 126:2[onaninso: dzadza, dzadzidwa, khuta]

DZALA (full)kuti chimwemwe chanu chidzale... Yoh 15:11[onaninso: dzadzidwa, dzadza]

DZANDIRA (stagger)nkumayenda ali dzandidzandi...Yob 12:25adzayamba kudzandira...Yer 25:16akuchita dzandidzandi...Yer 19:14

DZANJA (arm)ndidzakuombolani ndi dzanja...Eks 6:6kodi dzanja la Mulungu...Num 11:23iye pali dzanja...2 Mbir 32:8kulipulumutsa dzanja...Yob 26:2kodi uli nalo dzanja...Yob 40:9ndi dzanja lokwezeka...Mac 13:17[onaninso: mkono]

DZANJA (hand)dzanja lake lidzakhala lotsutsana...Gen 16:12dzanja kulipa dzanja...Eks 21:24dzanja la Mulungu linavutadi...1 Sam 5:11namlimbitsa dzanja lake mwa...1 Sam 23:16uza anatambasula dzanja...2 Sam 6:6tigwe m’dzanja la Yehova...2 Sam 24:14dzanja lokoma la Mulungu...Ezara 8:18alole dzanja lake lindilikhe...Yob 6:9amatambasula dzanja lake...Yob 15:25dzanja lako lako lamanja...Yob 40:14dzanja lamanja lanu landigwiriziza...Mas 18:35dzanja lanu linandilemera ine...Mas 32:4m’dzanja lamanja lanu mudzala...Mas 48:10dzanja lanu likhale pa munthu...Mas 80:17dzanja langa lidzakhazikika naye...Mas 89:21khalani pa dzanja la manja...Mas 110:1m’dzanja lamanja lake...Miy 3:16wa mfumu uli m’dzanja la Yehova...Miy 21:1dzanja lako lichipeza...Mlal 9:10mtima wake uli kudzanja...Mlal 10:2osapumitsa dzanja lako...Mlal 11:6dzanja lamanzere lake...Nyi 8:3dzanja langa linakhazika...Yes. 48:13tiri ntchito ya dzanja lanu...Yes 64:8dzanja lako lamanja likulakwitsa...Mat 5:30chimene lichita dzanja lako lamanja ...Mat 6:3ngati dzanja lako likulakwitsa...Marko 9:43alikukhala ku dzanja lamanja...Marko 14:62titalanditsidwa ku dzanja la adani...Luk 1:74alikuimirira pa dzanja la manja...Mac 7:55akhalanso pa dzanja la manja...Aro 8:34Paulo ndi dzanja langa...1 Akor 16:21ndakulemberani inu ndi dzanja langa...Agal 6:11khala pa dzanja la manja...Aheb 1:13anakhala pa dzanja la manja...Aheb 10:12m’dzanja lake la manja...Chiv 2:1[onaninso: manja, mkono, pafupi, yandikira]

DZENJE (ditch)onse awiri adzagwa m’dzenje...Mat 15:14

DZENJE (pit)iye timponye m’dzenje...Gen 37:20muli dzenje lakuya...Miy 22:14ndiye dzenje lakuya...Miy 23:27adzagwa mwini m’dzenje...Miy 28:10moyo wanga m’dzenje...Mali 3:53andende ako m’dzenje...Zek 9:11ngati idagwa m’dzenje...Mat 12:11[onaninso: chionongeko, manda, phompho]

DZENJE (snare)

Page 40: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mantha ndi dzenje zitifikira...Mali 3:47[onaninso: msampha]

DZIKO (country)turuka iwe m’dziko lako...Gen 12:1akuchokera kudziko lakutali...Miy 25:25nkunyamuka ulendo wa ku dziko lina...Mat 21:33mlendo kudziko lalonjezano...Aheb 11:9monga zililimu tikuona kuti ankafuna dziko lina...Aheb 11:16

DZIKO (earth)ndi dziko liri pansi panu...Deut 28:23a Mulungu adagwedeza dziko...Aheb 12:26musaononge msanga dziko...Chiv 7:3[onaninso: dziko lapansi]

DZIKO (world)pakuti dziko lonse ndi langa ndi kudzala kwake...Mas 50:12dziko lomwe lokhalamo anthu likhazikika...Mas 93:1onani dziko litsata pambuyo pake pa Iye...Yoh 12:19[onaninso: dziko lapansi, pansi]

DZIKO LA ANTHU AKUFA (hell)adzapita ku dziko la anthu akufa...Mas 9:17yotsikira ku dziko la anthu akufa...Miy 7:27[onaninso: gehena]

DZIKO LAPANSI (earth)adakhazika dziko lapansi pa...1 Sam 2:8kudzalamulira dziko lapansi...1 Mbir 16:33moyo wa munthu pa dziko lapansi...Yob 7:1adakoloweka dziko lapansi...Yob 26:7maziko a dziko lapansi...Yob 38:4dziko lapansi ndi zonse...Mas 24:1Mulungu ndiye mfumu ya dziko lapansi...Mas 47:9munadalitsa dziko lapansi...Mas 65:9musanalenge dziko lapansi...Mas 90:2dziko lapansi ligwedezeke...Mas 99:1uli pamwamba pa dziko lapansi...Mas 148:13pamene adakhazikitsa dziko lapansi...Miy 3:19dziko lapansi lisanalengedwe...Miy 8:23dziko lapansi limanjenjemera nazo...Miy 30:21dziko lapansi limakhalapobe...Mlal 1:4anthu otsika a padziko lapansi ...Yes 11:4dziko lapansi ndiye chopondapo...Yes 66:1dziko lapansi lidawala ndi ulemerero...Ezek 43:2ndidzagwetsa mdima pa dziko lapansi...Amo 8:9dziko lapansi ladzadzidwa...Hab 2:14pakuti Mulungu adzawapatsa dziko lapansi...Mat 5:5thambo ndi dziko lapansi zisanathe...Mat 5:18dziko la pansi lidzanthawa...Chiv 20:11latsopano ndi dziko lapansi latsopano...Chiv 21:1[onaninso: dziko]

DZIKO LAPANSI (world)Iyeyu adzaweruza dziko lapansi m’chilungamo...Mas 9:8ndipo munda ndiwo dziko lapansi...Mat 13:38anali m’dziko lapansi, ndi dziko linalengedwa ndi...Yoh 1:10pakuti Mulungu anakonda dziko lapansi...Yoh 3:16sanatume Mwana wake ku dziko lapansi kuti akaononge...Yoh3:17tidziwa kuti Mpulumutsi wa dziko lapansi ndi ...Yoh 4:42dziko lapansi silingathe kudana ndi inu...Yoh 7:7inu ndinu a dziko lino lapansi...Yoh 8:23ndipo dziko lapansi silindionanso Ine...Yoh 14:19ngati dziko lapansi lida inu, mudziwa kuti...Yoh 15:18mukadakhala a dziko lapansi, dziko lapansi likadakonda...Yoh15:19m’dziko lapansi mudzakhala nacho chivuto...Yoh 16:33sindipempherera dziko lapansi koma iwo amene...Yoh 17:9Atate wolungama dziko lapansi silinadziwa Inu...Yoh 17:25ndi dziko lapansi litsutsidwe ndi Mulungu...Aro 3:19

Mulungu anasankhula zopusa za dziko lapansi...1 Akor1:27

pakuti nzeru ya dziko lino lapansi ili yopusa...1 Akor 3:19mwa Iye dziko lapansi lipachikidwira ine...Agal 6:14ndi opanda Mulungu m’dziko lapansi...Aef 2:12atakonda dziko lino lapansi napita ku Tesalonika...2 Tim 4:10wosachitidwa mawanga ndi dziko lapansi...Yak 1:27bwenzi wa dziko lapansi aziika mdani wa Mulungu...Yak 4:4musakonde dziko lapansi kapena za mdziko lapansi...1 Yoh

2:15pakuti chilichonse cha m’dziko lapansi...1 Yoh 2:16ndipo dziko lapansi lipita ndi chilakolako chake...1 Yoh 2 :17mwa ichi dziko lapansi silizindikira ife...1 Yoh 3:1mwa ichi alankhula monga ochokera m’dziko lapansi...1 Yoh

4:5tili ife m’dziko lino lapansi...1 Yoh 4:17[onaninso: dziko, pansi]

DZINA (name)ndipo adatama dzina la...Gen 13:4dzina lako ndi Yakobo...Gen 35:10ili ndi dzina langa nthawi...Eks 3:15amene atchula pachabe dzina...Eks 20:7akutchulani dzina la Yehova...Deut 28:10dzina iri la ulemerero ndi...Deut 28:58anga otchedwa dzina langa...2 Mbir 7:14ndipo adzasowa dzina...Yob 18:17dzina lanu liposadi...Mas 8:1iwo akudziwa dzina lanu...Mas 9:10dzina lake la ulemerero...Mas 72:19dzina lake limveka mwa...Mas 76:1maufumu osaitana pa dzina...Mas 79:6dzina lanu patsani ulemerero...Mas 115:1koposa dzina lanu...Mas 138:2ndi kuyamika dzina lanu...Mas 138:3dzina la Yehova ndilo...Miy 18:10dzina la mwana wake ndani...Miy 30:4mwainu nokha tidzathula dzina...Yes 26:13dzina langa ndi lomweli...Yes 42:8udzatchedwa dzina latsopano...Yes 62:2wathu wachikhalire ndi dzina...Yes 63:16amene aitana dzina lanu...Yes 64:7wonse m’dzina la Mulungu...Mika 4:5adzaitana dzina langa...Zek 13:9dzina langa lidzakhala lalikuru...Mal 1:11inu akuopa dzina langa...Mal 4:2udzamutcha dzina lake Yesu...Mat 1:21dzina lanu liyeretsedwa...Mat 6:9sitinanenera mau m’dzina lanu...Mat 7:22mneneri pa dzina la mneneri...Mat 10:41akunja adzakhulupirira dzina...Mat 12:21atatu asonkhana m’dzina la langa...Mat 18:20ambiri adzafika m’dzina langa...Mat 24:5dzina lako ndani...Marko 5:9dzina lake la namwaliyo...Luk 1:27dzina lake ndi Yohane...Luk 1:63nadzalitaya dzina lanu...Luk 6:22kwa iwotu okhulupirira dzina...Yoh 1:12akadza wina dzina lake...Yoh 5:43dzina lake linalimbikitsa...Mac 3:16palibe dzina lina pansi...Mac 4:12kunyozedwa chifukwa cha dzinalo...Mac 5:41nampatsa dzina limene liposa...Afil 2:9chitani zonse m’dzina la...Akol 3:17adalowa dzina lakuposa...Aheb 1:4dzina lokomali muitanidwa...Yak 2:7pa dzina la Khristu...1 Pet 4:14ndipo ugwira dzina...Chiv 2:13dzina lakuti uli ndi moyo...Chiv 3:1akukhala nalo dzina...Chiv 14:1wosalemekeza dzina lanu...Chiv 15:4ali nalo dzina lolembedwa...Chiv 19:12

Page 41: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

DZINJA (summer)muzindikira kuti dzinja layandikira...Mat 24:32[onaninso: chilimwe]

DZINO (tooth)dzino kulipa dzino...Eks 21:24kudya ndi dzino lowawa...Miy 25:19dzino kulipa dzino...Mat 5:38

DZIRA (egg)choyera chadzira...Yob 6:6kapena atamupepha dzira...Luk 11:12

DZIWA (acknowledge)Mulungu anadziwa...Eks 2:25[onaninso: vomera, vomereza, zindikira]

DZIWA (acquainted)mumadziwa njira...Mas 139:3ndiwodziwa...Yes 53:3

DZIWA (understand)ochenjera m’kudziwa...Dan 1:4ndipo ndingadziwe zinsinsi...1 Akor 13:2[onaninso: dziwitsa, mvera, mvetsetsa, nzeru, zindikira]

DZIWE (pool)kukhala chidziwe cha madzi...Yes 41:18dziweli lili pafupi ndi...Yoh 5:2

DZIWITSA (teach)mutidziwitse kuwerenga masiku...Mas 90:12[onaninso: langiza, phunzitsa]

DZIWITSA (understand)makolo athu sanadziwitsa zodabwitsa...Mas 106:7[onaninso: dziwa, mvera, mvetsetsa, nzeru, zindikira]

DZOLA (anoint)m’malire anu onse osadzola...Deut 28:40nuvale zovala zapamaliro osadzola mafuta...2 Sam 14:2dzola mutu wako ndi kusamba nkhope yako...Mat 6:17[onaninso: dzoza, paka]

DZOMBE (caterpillar)ndi dzombe ntchito yao...Mas 78:46

DZOMBE (locust)ndi chosiya dzombe...Yow 1:4chimbalanga, dzombe lidachidya...Yow 1:4

DZOMBE (locusts)kuchuluka kwao ngati dzombe...Ower 7:12linadza dzombe ndi mphuchi...Mas 105:34dzombe liribe mfumu...Miy 30:27chakudya chake chinali dzombe...Mat 3:4nadya dzombe ndi uchi...Marko 1:6mudatuluka dzombe padziko...Chiv 9:3

DZOZA (anoint)ndi ana ake omwe ndi kuwadzoza...Eks 28:41ndipo udzandidzozere iye amene ndidzakuchulira...1 Sam 16:3mwandidzoza mutu wanga mafuta...Mas 23:5dzozani mafuta chikopa...Yes 21:5ndi kudzoza malo opatulikitsa...Dan 9:24anandidzozeratu thupi langa ku kuikidwa m’manda...Marko

14:8anagula zonunkhira kuti akadze kumdzoza Iye...Marko 16:1[onaninso: dzola, paka]

DZOZA (anointed)pakuti Yehova wandidzoza...Yes 61:1awiri odzozedwa aja...Zek 4:14chifukwa chake wandidzoza...Luk 4:18simunadzoza mutu wanga...Luk 7:46Mariya uja anadzoza Ambuye...Yoh 11:2amene mudamdzoza...Mac 4:27natidzoza ife, ndiye Mulungu...2 Akor 1:21[onaninso: dzozedwa]

DZOZEDWA (anointed)zoonadi, wodzozedwa wa Yehova...1 Sam 16:6kuononga wodzozedwa wa Yehova...2 Sam 1:14chifukwa cha kutemberera wodzozedwa...2 Sam 19:21naonetsa chifundo wodzozedwa...2 Sam 22:51musakhudze odzozedwa anga...1 Mbir 16:22apulumutsa wodzozedwa wake...Mas 20:6awiri odzozedwa aja...Zek 4:14[onaninso: dzoza]

DZUDZULA (corrects)amene Mulungu am’dzudzula...Yob 5:17Yehova adzudzula omwe amawakonda...Miy 3:12

DZUDZULA (rebuke)adzakudzudzulani ndithu mukachita tsankhu...Yob 13:10ndi kudabwa pa kudzudzula kwake...Yob 26:11aonongeka pa kudzudzula kwa nkhope yanu...Mas 80:16pa kudzudzula kwanu anathawa...Mas 104:7akandidzudzula ndidzakuyesa mafuta a pamutu...Mas 141:5tembenukani pamene ndikudzudzulani...Miy 1:23usadzudzule wonyoza kuti angakude...Miy 9:8chidzudzulo chilowa m’kati mwa wozindikira...Miy 17:10chidzudzulo chomveka chiposa chikondi chobisika...Miy 27:5kumva chidzudzulo cha anzeru kupambana kumva...Mlal 7:5nadzadzudzula amitundu amphamvu ali kutali...Mika 4:3akachimwa mbale wako umdzudzule...Luk 17:3Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu...Luk 19:39mkulu usamdzudzule komatu umdandaulire...1 Tim 5:1iwo akuchimwa uwadzudzule pamaso pa onse...1 Tim 5:20mwa ichi uwadzudzule mokaripa kuti...Tit 1:13koma anati Ambuye akudzudzule...Yuda 9onse amene ndiwakonda ndiwadzudzula ndi kuwalanga...Chiv

3:19

DZUKA (aroused)ndipo Yosefe atadzuka...Mat 1:24[onaninso: ipsa mtima]

DZULO (yesterday)ndife adzulodzulo...Yob 8:9ndi yemweyo dzulo...Aheb 13:8

DZUWA (sun)choncho dzuwa lidaima...Yos 10:13anu akhale ngati dzuwa...Ower 5:31ngakhale mpadzuwa pomwe...Yob 8:16Mulungu adamangira dzuwa...Mas 19:4Chauta ndiye dzuwa...Mas 84:11dzuwa silidzakupweteka...Mas 121:6dzuwa kuti lidzilamulira...Mas 136:8ako akaona dzuwa...Mlal 11:7dzuwa kuwala mwezi...Mlal 12:2wowala ngati dzuwa...Nyi 6:10udzawala ngati dzuwa...Yes 30:26chithunzithunzi chimene dzuwa...Yes 38:8sipadzafikanso dzuwa...Yes 60:19amene amawalitsa dzuwa...Yer 31:35dzuwa ndi mwezi zikuchita...Yow 2:10dzuwa lidzasanduka mdima...Yow 2:31dzuwa ndi mwezi zidangoti...Hab 3:11amawalitsa dzuwa lao...Mat 5:45

Page 42: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

dzuwa litangoti bii...Luk 23:45dzuwa lili ndi kuwala...1 Akor 15:41dzuwa likulowereni...Aef 4:26dzuwa lidangoti bii...Chiv 6:12sadzaombedwanso ndi dzuwa...Chiv 7:16choti dzuwa kapena mwezi...Chiv 21:23

EEBALA (Ebal)

phiri la ku Samariya...Deut 27:12,13miyala ya chilamulo inasankhidwapo...Deut 27:1-8;Yosw8:30-35

EBEDEMELEKI (Ebed-melech)wantchito wa kunyumba ya mfumu; anampulumutsaYeremiya...Yer 38:7-13analonjezedwa chitetezo kuchokera kwa Mulungu...Yer39:15-18

EBENEZERI (Ebenezer)malo omwe a Israeli anagonjetsedwera...1 Sam 4:1-10likasa linatengedwako...1 Sam 5:1malo a mwala wa chikumbutso...1 Sam 7:10,12

EBERI (Eber)chidzukulu cha Semu chotchuka...Gen 10:21-24;1 Mbir 1:25kholo la: Ahebri...Gen 11:16-26Aarabu (Arabians) ndi Aarame (Arameans)...Gen 10:25-30kholo la Khristu...Luk 3:35

EDENI (Eden)malo oyamba a mtundu wa anthu...Gen 2:8-15Ziyoni anakhala ngati malo amenewa ...Yes 51:3wotchedwa “munda wa Mulungu...Ezek 28:13

EDEREI (Edrei)mzinda waukuru wa Basani...Deut 3:10malo akugonjetsedwa kwa Ogi...Num 21:33-35

EDOMU (Edom)dzina lopatsidwa kwa Esau...Gen 25:30dziko la Esau; lotchedwa Seiri...Gen 32:3wotchedwa Edomu ndi Idumeya...Marko 3:8anthu ake anatembereredwa...Yes 34:5,6

EFESI-DAMIMU (Ephes-dammim)malo omwe Afilisti anamangapo zithando zao...1 Sam 17:1wotchedwa Pasidamimu...1 Mbir 11:13

EFESO (Ephesus)Paulo anakachezako...Mac 18:18-21zozizwa zinachitikako...Mac 19:11-21Demetrio anayambitsa chiwawa...Mac 19:24-29akulu ampingo ake anayankhulidwa ndi Paulo ku Mileto...Mac20:17-38kalata inatumizidwako...Aef 1:1malo a mpingo umodzi mwa mipingo isanu ndi iwiri...Chiv1:11

EFURATA (Ephrathah)dzina lake la Betelehemu...Rut 4:11uneneri wake...Mika 5:2

EFUREMU (Ephraim)mwana wotsiriza wa Yosefe...Gen 41:52analandira madalitso a Yakobo...Gen 48:8-20— fuko lake;linakangana ndi Gideoni...Ower 8:1-3linakangana ndi Yefita...Ower 12:1-4ufumu wotsogolera wa Israeli...Yes 7:2-17Mulungu anaipidwa nao chifukwa cha tchimo...Hos 12:7-14anthu ake ambiri analowa fuko la Yuda...2 Mbir 15:8,9

ukapolo wake, unaloseledwa...Hos 9:3-17linalonjezedwa Mesiya...Zek 9:9-13mwana wamng’ono wa Yosefe...Gen 41:52analandira madalitso a Yakobo...Gen 48:8-20fuko lake:linaloseredwa...Gen 48:20anapatsidwa malo...Yos 16:1-10linathandiza Debora...Ower 5:14,15linathandiza Gideoni...Ower 7:24,25

EFURONI (Ephron)Muhiti yemwe anagulitsa makipera kwa Abrahamu...Gen

23:8-20

EHUDI (Ehud)mwana wa mwamuna wa Gera...Ower 3:15ananyonga Egiloni...Ower 3:16-26

EJIPITO (Egypt)Abramu anapitako...Gen 12:10kumene Yosefe anagulitsidwira...Gen 37:28,36kumene Yosefe anakhala mtsogoleri...Gen 39:1-4Ahebri anapitako...Gen 46:5-7Ahebri (Ayuda) anazunzidwako...Ekso 1:15-22miriri inachitikamo...Eks 7-11Aisraeli anachokamo...Eks 12:31-33ankhondo ake anaonogedwa...Eks 14:26-28ananeneredwa uneneri...Gen 15:13;Yes 19:18-25;Ezek29:14,15;30:24,25;Mat 2:15

EKERONI (Ekron)mzinda wa Afilisti...Yos 13:3wolandidwa ndi Yuda...Ower 1:18wopatsidwa kwa Dani...Yos 19:40, 43likasa linatumizidwako...1 Sam 5:10unaneneredwa zoipa ndi aneneri...Yer 25:9,20

ELA (Elah)mfumu ya Israeli...1 Maf 16:6,8-10

ELAMU (Elamites)zidzukuru za Semu...Gen 10:22za chionongeko chake...Yer 49:34-39anali mu ufumu wa Perisiya...Ezara 4:9Ayuda ochokera kumeneku analipo pa tsiku la Pentekoste...Mac2:9

ELATI (Elath)gombe pa nyanja yofiira...1 Maf 9:26womangidwa ndi Azariya...2 Maf 14:21,22wogonjetsedwa ndi Aasiriya...2 Maf 16:6wotchedwanso Eziyoni-Gebere...2 Mbir 8:17

ELEAZARA (Eleazar)mwana wa Aaroni;analowa unsembe...Eks 6:23,25;28:1;Lev 10:6,7;Num3:32;20:25-28Yos 14:1;24:33

ELI (Eli)amagwira ntchito ku Silo...1 Sam 1:3anamdalitsa Hana...1 Sam 1:12-19anakhala omuyang’anira Samuele...1 Sam 1:20-28Samuele anatumikira Chauta pamaso pake...1 Sam 2:11ana ake...1 Sam 2:12-17anadzudzula ana...1 Sam 2:22-25anadzudzulidwa ndi munthu wa Mulungu ...1 Sam 2: 27-36anamlangiza Samuele...1 Sam 3:1-18imfa yake...1 Sam 4:15-18

ELIBETELI (El bethel)malo omwe Yakobo anamanga guwa la nsembe...Gen 35:6,7

Page 43: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ELIFAZI (Eliphaz)m’modzi wa anzake a Yobu...Yob 2:11anamdzudzula Yobu...Yob 4:1,5anakhululukidwa ...Yob 42:7-9

ELIHU (Elihu)mbale wa Davide...1 Mbir 27:18wotchedwa Eliabu...1 Sam 16:6— yemwe anadana ndi Yobu ndi anzake...Yob 32:2,4-6

ELIKANA (Elkanah)atate ake a Samuele...1 Sam 1:1-23— mwana wamwamuna wa Kora...Eks 6:24anathawa chilango...Num 26:11

ELIMASI (Elymas)dzina la chi Arabiya la Barayesu, mneneri wonyenga...Mac13:6-12

ELIMELEKI (Elimelech)mwamuna wake wa Naomi...Rut 1:1-3;2:1,3;4:3-9

ELINATI (Elnathan)tate a Nehusita...2 Maf 24:8anapita ku Ejipito...Yer 26:22anapempha kwa mfumu...Yer 36:25

ELISA (Elisha)anasankhidwa kulowa m’malo mwa Eliya; anamtsatira Eliya...1Maf 19:16-21anaonerera za kutengedwa kwa Eliya; analandira Mzimu,chofundira cha Eliya...2 Maf 2:1-18anachita zodabwitsa...2 Maf 2:19-25;4:1-6:23ananenera chigonjetso pa Moabu; zinakwaniritsidwa...2 Maf3:11-27ananenera kutha kwa ukapolo ndipo zinakwaniritsidwa...2 Maf

7ananenera za imfa ya Benihadadi...2 Maf 8:7-15anatumiza kapolo wake kukadzoza Yehu...2 Maf 9:1-3mau ake omaliza ndi imfa; chozizwa chinachitika ndi mafupaake...2 Maf 13:14-21

ELIYA (Elijah)anadzudzula Ahabu; anapita kukabisala; anadyetsedwa ndimakwangwala...1 Maf 17:1-7anakhala ndi mai wa masiye; anamchitira zodabwitsa...1 Maf17:8-24anatumiza uthenga kwa Ahabu; napha aneneri a Baal...1 Maf18:1-40anabweretsa mvula...1 Maf 18:41-45anathawa kuchokera kwa Yezebele; anadyetsedwa ndiangelo...1 Maf 19:1-8analandira vumbulutso kuchokera kwa Mulungu...1 Maf19:9-18anamlangiza Ahabu...1 Maf 21:15-29anadzudzula Ahaziya; moto unanyeketsa magulu ankhondootumizidwira iye...2 Maf 1:1-16anatengedwa kunka kumwamba...2 Maf 2:1-15anaonekera ndi Khristu pa kusinthika maonekedwe kwaYesu...Mat 17:1-4anaikidwa m’gulu limodzi ndi Yohane mbatizi... Mal 4:5,6;Luk1:17

ELIYABU (Eliab)mbale wa Davide...1 Sam 16:5-13anamenya nkhondo mu gulu la nkhondo la Saulo...1 Sam 17:13anamunyoza Davide...1 Sam 17:28-29

ELIYAKIMU (Eliakim)mwana wa Hilikiya...2 Maf 18:18anakambirana ndi kazembe wa Senakeribu...Yes 36:4,11-22anatumidwa kwa Yesaya...Yes 37:2-5

anavekedwa ufumu...Yes 22:20-25— mwana wamwamuna wa mfumu Yosiya...2 Maf23:34dzina lake linasinthidwa kukhala Yehoyakimu...2 Mbir 36:4

ELIYASIBU (Eliashib)wamkulu wansembe...Neh 12:10adamanga chipata cha nkhosa ...Neh 3:1,20,21adagwirizana ndi achikunja...Neh 13:4,5,28

ELIZABETI (Elizabeth)mkazi wouma (wosabereka) wa Zakariya...Luk 1:5-7anakhala ndi pakati pa mwana wamwamuna...Luk1:13,24,25anapereka ulemu kwa Mariya...Luk 1:36:45mai ake a Yohane mbatizi...Luk 1:57-60

ELIZAFANI (Elizaphan)mfumu ya Akohati...Num 3:30anakhala mutu wa banja...1 Mbir 15:5,8banja lake linayeretsedwa...2 Mbir 29:12-16

EMAUSI (Emmaus)mzinda womwe uli pafupi ndi Yerusalemu...Luk 24:13-18

ENGEDI (En Gedi)unazazidwa ndi Aamoni...Gen 14:7unapatsidwa kwa Yuda...Yos 15:62,63malo obisalira a Davide...1 Sam 23:29okhala ndi minda ya mphesa...Nyi 1:14

ENIHAKORE (Enhakkore)kasupe wachozizwa...Ower 15:14-19

ENIROGELE (Enrogel)chitsime kunja kwa Yerusalemu...2 Sam 17:17mpando wa zolinga za Adoniya...1 Maf 1:5-9

ENOKI (Enoch)tate ake a Matusela...Gen 5:21anayenda ndi Mulungu...Gen 5:22anatengedwa kupita kumwamba...Gen 5:24uneneri wake unanenedwa monga chitsanzo...Yuda 14,15

EPAFRA (Epaphras)mtsogoleri ku mpingo wa ku Kolose...Akol 1:7,8azunzika monga wa m’ndende ku Roma...Fil 23

EPAFRODITO (Epaphroditus)wotumikira wochokera ku Filipi...Afil 2:25-27anabweretsa mphatso kwa Paulo...Afil 4:18

ERASITO (Erastus)m’nzake wa Paulo ku Efeso...Mac 19:21,22;2 Tim 4:20msungi chuma wa ku Korinto...Aro 16:23

ERE (Er)mwana wamwamuna wa Yuda...Gen 38:1-7;46:12

ESARAHADONI (Esarhaddon)mwana wamwamuna wa Senakeribu; mfumu ya Asiriya

(681-669BC)...2 Maf 19:36,37

ESAU (Esau)mwana wokondedwa wa Isake...Gen 25:25-28anagulitsa ukulu wake...Gen 25:29-34analandidwa madalitso, anafuna kupha Yakobo...Gen 27anagwirizananso ndi Yakobo...Gen 33:1-17zidzukulu zake...Gen 36

ESIBAALA (Esh-baal)mwana wa Saulo...1 Mbir 8:33

Page 44: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ESIKOLO (Eshcol)chigwa chomwe chinali pafupi Heburoni...Num 13:22-27;Deut1:24

ETAMU (Etam)tanthe lomwe Samsoni anapumulapo...Ower 15:8-19

ETIOPIYA (Ethiopia)onani Kusi (Cush)mdani wa Israeli ndi Yuda...2 Mbir 12:2,3;14:9-15;Yes43:3;Dan 11:43mauneneri otsutsana nalo...Yes 20:1-6;Ezek 30:4-9

EVILI-MERODAKI (Evil-merodach)mfumu ya ku Babiloni (562-560 BC)...2 Maf 25:27-30

EZARA (Ezra)Mlembi, wansembe ndinso yemwe anakhazikitsanso anthuochokera ku ukapolo, abatumidwa ndi Aritasasta, Ezra 7anabwerera ndi anthu kuchokera ku ukapolo kupita kuYerusalemu...Ezara 8atsogolera anthu obwerera ku ukapoloanawerenga malamulo...Neh 8anathandiza kupereka linga...Neh 12:27-43

EZEKIELI (Ezekiel)anatumizidwa kwa Israeli woukira...Ezek 2;3ananenera pakuwonetsa zintchito, kuzingidwakwaYerusalemu...Ezek 4chionongeko cha Yerusalemu...Ezek 5ukapolo wa Yuda ...Ezek 12:1-20chionongeko cha kachisi...Ezek 24:15-27Masomphenya a:ulemelero wa Mulungu...Ezek 1:4-28zoipitsa...Ezek 8:5-18chigwa cha mafupa ouma...Ezek 37:1-14nthawi za Mesiya...Ezek 40-48mtsinje wa moyo ...Ezek 47:1-5mafanizo. Ezek 15-17;19;23;24

EZIYONI-GEBERE (Ezion-gebermzinda pa gombe la nyanja yofiira...1 Maf 9:26malo omwe Aisraeli anamanga zithando zao...Num 33:35doko la chitetezo la Israeli, 1 Maf 22:48

FFAFANIZA (blot)

sadanena kuti adzafafaniza...2 Maf 14:27ndipo mufafanize mphulupulu...Mas 51:9sindidzafafaniza ndithu dzina lake...Chiv 3:5

FAFANIZA (blotted)ine ndifafaniza monga mtambo...Yes 44:22[onaninso: fafanizidwa]

FAFANIZIDWA (blotted)afafanizidwe m’buku la moyo...Mas 69:28kuti afafanizidwe machimo anu...Mac 3:19[onaninso: fafaniza]

FAFANIZIKA (extinguished)masiku anga afafanizika...Yob 17:1[onaninso: zimidwa]

FANA (equity)kukhala wofana ndi Mulungu...Afil 2:6[onaninso: lunjika, ongoka, onongeka]

FANIZIDWA (conformed)afanizidwe ndi chifaniziro cha...Aro 8:29musafanizidwe ndi makhalidwe a pansi...Aro 12:2

pofanizidwa ndi imfa yake...Afil 3:10lifanane nalo thupi lake la ulemerero...Afil 3:21

FANIZO (parable)ndidzakusimbirani fanizo...Mas 78:2lankhula nao kanthu wopanda fanizo...Mat 13:34fanizoli mukupemphera ife tokha...Luk 12:41

FANIZO (parables)mudzamvetsa bwanji fanizo...Marko 4:13[onaninso: mafanizo]

FANO (idol)kapena kupembedza fano...Yes 66:3ozolowera fano kufikira tsopano...1 Akor 8:7yoperekedwa nsembe kwa fano...1 Akor 10:19

FARAO (Pharaoh)mafumu a ku Ejipito, nthawi ya:Abrahamu...Gen 12:15-20Yosefe...Gen 40;41Mose ali mnyamata...Eks 1:8-11ulendo wotuluka Ejipito (Eksodo)...Eks 5-14Solomoni...1 Maf 3:1;11:17-20Afarao ena...1 Maf 14:25,26;2 Maf 17:4;18:21;19:9;23:29;Yer44:30

FATSA (gentle)lilime lofatsa lithyola fupa...Miy 25:15ndiri wofatsa ndi wodzichepetsa...Mat 11:29tinakhala ofatsa pakati pa inu...1 Ates 2:7apewe kukangana, akhale ofatsa...Tit 3:2okhao amene ali abwino ndi ofatsa ai...1 Pet 2:18cha Mzimu, wofatsa ndi wachete...1 Pet 3:4

FATSA (humility)ofatsa inu nonse a m’dziko...Zef 2:3iwo akutsutsana mofatsa...2 Tim 2:25[onaninso: chifatso, kudzichepetsa]

FELIKISI (Felix)bwanamkubwa wa ku Yudeya, kumene kalata inafikira...Mac23:24-30Paulo anaziikira kumbuyo pamaso pake...Mac 24:1-27

FENESIYA (Phoenicia)dera la Meditereniyani kuphatikizirapo mizinda ya Tolemaisi,Taya, Zerefati ndi Sidoni anachitiridwa umboni ndi akhristuoyambirira...Mac 11:19Yesu analalikirako...Mat 15:21

FESA (sow)adafesa mbeu m’minda...Mas 107:37amene amafesa akulira...Mas 126:5woyang’ana mphepo sadzafesa...Mlal 11:4mudzifesere mchilungamo...Hos 10:12mbeu imene imafesa...1 Akor 15:36[onaninso: bzyala]

FESA (sown)inde sanaokedwe inde sanafesedwe...Yes 40:24mwafesa zambiri...Hag 1:6ife tidafesa zabwino...1 Akor 9:11lifesedwa m’mnyozo, liukitsidwa mu ulemelero...1 Akor 15:43odzetsa mtendere anafesa...Yak 3:18[onaninso: bzyala]

FESITO (Festus)bwanankubwa wa ku Yudeya...Mac 24:27Paulo anaziteteza pamaso pake...Mac 25:1-22

FIKA (comes)pamenepo chimaliziro chidzafika...1 Akor 11:26

Page 45: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: idza]

FIILA (red)chingwe chofiira pawindo...Yos 2:18ili ngati mbota yofiira...Nyi 4:3ngakhale zoipa zanu zili zofiira...Yes 1:18pa chilombo chofiira...Chiv 17:3

FILADELFIYA (Philadelphia)mzinda wa ku Lidiya, mpingo unakhazikitsidwapamenepa...Chiv 1:11

FILEMONI (Philemon)mkhristu wa ku Kolose yemwe Paulo akulembera...Fil 1Paulo anampempha kuti amulandire Onesimo...Fil. 9-20

FILIPI (Philipp)mzinda wa ku Masedoniyaunatchulidwa dzina limeneli chifukwa cha Filipo wa kuMasedoniyaPaulo anakachezako...Mac 16:12;20:6

FILIPO (Philip)mwana wa Herodi wotchuka...Mat 14:3— m’modzi wa atumwi khumi ndi awiri...Mat 10:3anam’bweretsa Natanieli kwa Ambuye...Yoh 1:43-48anayesedwa ndi Yesu...Yoh 6:5-7amawauza Agriki za Khristu...Yoh 12:20-22— m’modzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:5wotchedwa mlaliki...Mac 21:8analalikira ku Samariya...Mac 8:5-13anatsogolera nduna ya ku Etiopiya kwa Khristu...Mac 8:26-40

FILISITIYA (Philistia)dziko la Afilisti...Gen 21:32,34;Yosw 13:2;Mas 60:8

FINEHASI (Phinehas)chidzukulu cha Aroni...Num 25:1-18;Mas 106:30,31anathetsa mkangano wa guwa la chikumbutso...Yos 22:11-32— mwana wamng’ono wa Eli; sanagwire bwino ntchitoyake...1 Sam 1:3;2:12-17,22-36anaphedwa ndi Afilisti...1 Sam 4:11,17

FOOKA (fail)ndi mtima wanga zingafooke...Mas 73:26[onaninso: lephera]

FOOKA (feeble)panalibe amene adafooka...Mas 105:37tsono manja anu ofooka...Aheb 12:12[onaninso: kutha mphamvu, lefuka, onda]

FOOKA (weak)ndidzasanduka wofooka...Ower 16:7ine lero ndafooka…2 Sam 3:39pakuti ndine wofooka...Mas 6:2amalimbitsa wofooka...Yes 40:29ngakhale wofooka anene...Yow 3:10langokhala lofooka ndi thupi...Mat 26:41chikhulupiriro chake nchofooka...Aro 14:1anthu amaziyesa zofooka...1 Akor 1:27ife ndife ofooka...1 Akor 4:10ali ndi chikhulupiriro chofooka...1 Akor 9:22inu akudwala, akufooka...1 Akor 11:30pamene ndili wofooka...2 Akor 12:10ndife ofooka...Aro 8:26chifukwa cha zofooka zathu...Aheb 4:15

FOTA (fade)tikufota ngati masamba...Yes 64:6ndipo tsamba lidzafota...Yer 8:13wachuma adzafota mayendedwe...Yak 1:11

chosadetsa ndi chosafota...1 Pet 1:4

FOTA (fades)udzu unyala, duwa lifota...Yes 40:7

FOTA (wither)masamba ake safota...Mas 1:3amafota ngati masamba...Mas 37:2masamba ake sadzafota...Ezek 47:12maluwa amafota...Yes 40:7

FOTOKOZA (declare)ndani adzafotokoza nthawi ya...Yes 53:8[onaninso: fotokozera, lalikira]

FOTOKOZA (explain)ndipo ndinafotokozera amatsenga...Gen 41:24mutifotokozere ife fanizoli...Mat 15:15koma nzovuta kufotokoza...Aheb 5:11[onaninso: tanthauzira]

FOTOKOZERA (declare)ndipo ndidzafotokozera zonse...Mas 66:16[onaninso: fotokoza, lalikira]

FOTOKOZERA (disclose)ndidzafotokozera chophiphiritsa...Mas 49:4

FRIGIYA (Phrygia)Ayuda ochokera kumeneku analipo patsiku la Pentekoste...Mac2:1,10Paulo anapitako kawiri...Mac 16:6

FUKO (tribe)ukhale fuko la cholandira chanu...Mas 74:2anali a fuko lina...Aheb 7:13wa m’fuko la Yuda...Chiv 5:5anthu a fuko lililonse...Chiv 5:9

FULUMIZA (compels)ndi mzimu wa mkati mwanga andifulumiza...Yob 32:18[onaninso: kakamiza]

FUMBATULA (open)mufumbatula dzanja lanu...Mas 104:28[onaninso: tsegula, tsekuka, tsekula]

FUMBI (dust)amene angawerenge fumbi...Gen 13:16ine ndine fumbi ndi phulusa...Gen 18:27Yakobo zochuluka ngati fumbi...Num 23:10ndikulapa podzithira fumbi...Yob 42:6kodi ine nditasanduka fumbi...Mas 30:9muwasandutse ngati fumbi...Mas 83:13nachitira chifundo fumbi lake...Mas 102:14kuti ife ndife fumbi...Mas 103:14musanse fumbi la kumapazi...Mat 10:14[onaninso: dothi]

FUNA (desires)kodooko komwe afunako...Mas 107:30[onaninso: khumba, zolakolako]

FUNA (need)sindikufuna iwe...1 Akor 12:21ndipo pamzinda sipafunika dzuwa...Chiv 21:23[onaninso: sowa]

FUNA (seek)koma iwo andifuna ine tsiku ndi tsiku...Yes 58:2usandifunire zoterezi...Yer 45:5muchite zimene ine ndifuna...Amo 5:4

Page 46: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: funafuna]

FUNA (will)kufuna kwanu kuchitidwe...Mat 6:10Atate anga akumwamba akufuna...Mat 7:21bambo ake ankafuna...Mat 21:31osati zimene ndikufuna...Luk 22:42sindichita zimene ndifuna...Yoh 5:30kudzachita zofuna za iye...Yoh 6:38chofuna iye amene wandituma...Yoh 6:39kuchita kufuna kwa Mulungu...Yoh 7:17anadzifunira yekha ulemu...Yoh 7:18ndimafuna kuchita zabwino...Aro 7:18kudziwa zimene Mulungu afuna...Aro 12:2muzifuna ndi kutha...Afil 2:13zonse zimene iye afuna...Akol 1:9monga momwe iye ankafunira...Aheb 2:4ndichite zimene mukufuna...Aheb 10:9muzichita zimene iye afuna...Aheb 13:21wochita zimene Mulungu afuna...1 Yoh 2:17[onaninso: chifuniro]

FUNA (willing)ndi mtima wofuna...Eks 35:5ngati inu muli ofuna ndi omvera...Yes 1:19chabwino ndikufuna, chira...Mat 8:3mtima ndiye ukufunitsitsadi...Mat 26:41mtima ndiye ukufunitsitsadi...Marko 14:38safuna kuti ena aonongedwe...2 Pet 3:9

FUNA (willingly)chosafuna mwini...Aro 8:20mofuna inu nokha...1 Akor 9:17koma mofuna nokha…1 Pet 5:2

FUNA (wills)amene mwanayo akufuna...Mat 11:27zimene munthu azifuna...Aro 9:16[onaninso: lola]

FUNAFUNA (hunt)mukufunafuna moyo wanga...1 Sam 24:11mufuna kukola mitima...Ezek 13:18[onaninso: saka]

FUNAFUNA (seek)inu mudzamfunafuna Chauta...Deut 4:29ndikufunafuna nkhope yanga...2 Mbir 7:14ndi mtima wonse kufunafuna...2 Mbir 19:3muzifunafuna nkhope yanga...Mas 27:8Mulungu wanga ndimakufunafunani...Mas 63:1anthu ondifunafuna...Miy 8:17funafuna chilungamo...Yes 1:17zotayika ndizazifunafuna...Ezek 34:16anazifunafuna ndi anthu...Mat 6:32yambani mwafunafuna ufumu...Mat 6:33funafunani ndipo mudzapeza...Mat 7:7kudzafunafuna ndi kudzapulumutsa...Luk 19:10[onaninso: funa]

FUNDA (lukewarm)popeza uli wofunda...Chiv 3:16

FUNGO LOKOMA (aroma)atamva fungo lokomalo...Gen 8:21fungoli ndi lamoyo...2 Akor 2:16nsembe ya fungo lokondweretsa...Aef 5:2chopereka cha fungo lokoma...Afil 4:18

FUNGO LOKOMA (fragrance)fungo la zovala zako likumveka...Nyi 4:11guu ndi fungo la mafutawo...Yoh 12:3

tili ngati fungo labwino la Khristu...2 Akor 2:15

FUNITSITSA (desire)funitsitsani mphatso za uzimu...1 Akor 14:1[onaninso: chikhumbo, chilakolako, khumba, lakalaka]

FUNKHA (plunder)onse ofunkha zinthu...Yer 30:16wamphamvu nkufunkha chuma...Mat 12:29[onaninso: landa]

FUNKHA (plundered)mudalanda zofunkha...Mas 76:5awalanda ndikuwafunkhira...Yes 42:22udafunkha mitundu yambiri...Hab 2:8[onaninso: landa]

FUNSIRA (inquired)anafunsira kwa Yehova...Ower 20:27Davide anafunsira kwa Yehova...1 Sam 23:2kapena kufunsira kwa iye...Zef 1:6[onaninso: santhula]

FUPA (bone)uyu tsopano ndiye fupa...Gen 2:23fupa langa laumirira...Yob 19:20fupa kutsata fupa...Ezek 37:7

FUTUKA (depart)futuka pa zoipa nichite zabwino...Mas 34:14[onaninso: choka, patuka]

FUULA (cry)anthu akufuula chifukwa...Yob 35:9zifuulira kwa Mulungu...Mas 84:2kodi ndifuule chiyani...Yes 40:6pakati pa usiku panali kufuula...Mat 25:6[onaninso: lira]

FUULA (crying)mau a wofuula mchipululu...Mat 3:3[onaninso: kulira]

GGAALA (Gaal)

mwana wa Ebedi; anatukwana Abimeleki...Ower 9:26-41

GAASI (Gaash)phiri la Eferemu...Ower 2:9Yoswa anaikidwa pafupu ndi malo amenewa...Yos 24:30

GABATA (Gabbatha)malo oweruzira milandu a Pilato...Yoh 19:13

GABRIELE (Gabriel)m’ngelo wamkulu wotumikira, anamasulira masomphenya aDaniele...Dan 8:16-27anaonetsera uneneri wa milungu 70...Dan 9:21-27analengeza za kubadwa kwa Yohane...Luk 1:11-22analengeza za kubadwa kwa Khristu...Luk 1:26-38woimirira mkupezeka kwa Mulungu...Luk 1:19

GADI (Gad)mwana wamwamuna wa Yakobo kudzera mwa Zilipa...Gen30:10-11anadalitsidwa ndi Yakobo...Gen 49:19— fuko la Gadi:Anachita chiwerengero...Num 1:24,25dela lake...Num 32:20-36ukapolo wake...1 Mbiri 5:26— mneneri nthawi ya Davide...1 Sam 22:5uthenga wake kwa Davide...2 Sam 24:10-16

Page 47: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ananenedwanso ku Chivumbulutso...Chiv 7:5

GALAMUKA (awake)galamukani chisakasa ndi zeze...Mas 108:2galamuka mphepo ya kumpoto...Nyi 4:16[onaninso: dikira, khala maso, kumika, uka]

GALATIYA (Galatia)Paulo anakachezako...Mac 16:6;18:23Paulo analembera akhristu ake...Agal 1:1Petro analembera akhristu ake...1 Pet 1:1

GALETA (chariot)ndipo anagurura njinga za magaleta...Eks 14:25adangoona galeta lamoto...2 Maf 2:11ili ngati galeta lanu...Mas 104:3kayandikane nalo galetalo...Mac 8:29

GALILEYA (Galilee)uneneri wokhudzana nawo...Deut 33:18-23;Yes 9:1,2chilankhulo chake chosiyana ndi zilankhulo zina za maderaozungulira...Mat 26:73dera lomwe Herodi analamulira...Luk 3:1Khristu anafikako...Mat 2:22;4:12-25;26:32;27:55;Yoh 4:1,3

GALILEYA, NYANJA YA (Galilee sea of)malo azochitika zambiri m’moyo wa Khristu...Marko 7:31yotcheda Kinereti...Num 34:11kenaka inatchedwa Genesarete...Luk 5:1

GALIO (Gallio)bwanamkubwa wa chiroma wa ku Akiyaanakana umboni wabodza pa mulandu wa Paulo...Mac 18:12-17

GALU (dog)Davide kuti, kodi ndine galu...1 Sam 17:43akuuwa ngati galu...Mas 59:6chili ngati galu wodya masanzi...Miy 26:11ndiponi galu wamoyo...Mlal 9:4galu wabwerera ku masanzi ake...2 Pet 2:22

GALUKIRA (rebel)musagalukire Chauta...Num 14:9[onaninso: panduka, pikisana, ukira]

GALUKIRA (rebellion)kugalukira kuli ngati tchimo...1 Sam 15:23[onaninso: pandukira, ukira]

GAMALIELE (Gamaliel)mphunzitsi wachiyuda wotchuka...Mac 22:3wopatsidwa ulemu ndi anthu...Mac 5:34-39

GANIZA (think)mtima wake sukuganiza...Yes 10:7mumaganiza kuti mupezamo...Yoh 5:39kangatiganizitse kuti tingathe...2 Akor 3:5tingazipemphe kapena kuganiza...Aef 3:20[onaninso: yesa]

GANIZA (thinks)monga aganiza m’kati...Miy 23:7akuganiza kuti waimirira...1 Akor 10:12[onaninso: kumbukira, yesa]

GANIZA (thought)unali kuganiza kuti…Mas 50:21amaganizira zoipa...Mas 64:6ndinaganizira njira zanga...Mas 119:59mumazindikira maganizo...Mas 139:2monga momwe ndaganizira...Yes 14:24nafotokozera munthu maganizo ake...Amo 4:13

adayamba kuganiza...Luk 12:17ndinkaganiza mwachibwana...1 Akor 13:11[onaninso: yesa]

GATI (Gath)mzinda wa Afilisti...1 Sam 6:17likasa linatengedwerako...1 Sam 5:8Davide anathawirako...1 Sam 21:10-15Davide anathawirakonso...1 Sam 27:3-12unagonjetsedwa ndi kutengedwa ndi Davide...1 Mbir 18:1chionongeko chake chinaneneredwa mu uneneri...Amo 6:1-3dzina lake linakhala mwambi...Mika 1:10

GAWA (divide)gawani lilime lawo...Mas 55:9limagawana chuma ndi...Miy 16:19kuti andigawireko chuma changa...Luk 12:13muchigawane mwa inu nokha...Luk 22:17[onaninso: dula pakati, gawikana]

GAWA (distribute)nugawire osauka...Luk 18:22

GAWA (divided)mudagawa nyanja pakati...Neh 9:11ufumu wanu wagawidwa...Dan 5:28dziko lako adzaligawagawa...Amo 7:17[onaninso: gawanika, gawika, gawikana, gawira, lekana]

GAWANA (divides)akugawana zofunkha...Mas 68:12

GAWANA (share)okonda kugawana zinthu...1Tim 6:18[onaninso: dudukira, gawira]

GAWANIKA (cloven)ziboda zogawanika...Lev 11:3kapena zogawanika chiboda...Deut 14:7

GAWANIKA (divided)ufumu uliwonse ogawanika...Mat 12:25ufumu uliwonse wogawanika...Luk 11:17nyumba ikagawikana...Luk 11:17[onaninso: gawa, gawika, gawikana, gawira, lekana]

GAWIKA (divided)kodi Khristu wagawika?...Akor 1:13udagawika patatu...Chiv 16:19[onaninso: gawa, gawanika, gawikana, gawira, lekana]

GAWIKANA (divide)ndipo madziwo adagawikana...Eks 14:21[onaninso: dula pakati, gawa]

GAWIKANA (divided)kapena kugawikana maufumu...Ezek 37:22anthu asanu ogawikana...Luk 12:52tikugawikana nkukhala pa iwo...Luk 11:17[onaninso: gawa, gawanika, gawika, gawira, lekana]

GAWIKANA (division)la anthu lidagawikana...Yoh 7:43[onaninso: gawira]

GAWIRA (distributed)ndipo anagawira yense...Mac 4:35monga Ambuye wagawira...1 Akor 7:17

GAWIRA (divided)anawagawiradi ana ake...Luk 15:12

Page 48: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndalama zake nkumagawira onse...Mac 2:45[onaninso: gawa, gawanika, gawika, gawikana, lekana]

GAWIRA (division)napyoza kufikira kugawira moyo ndi...Aheb 4:12[onaninso: gawikana]

GAWIRA (share)anjala muziwagawirako...Yes 58:7agawireko mphunzitsi wake...Agal 6:6kuchitira chokoma ndi kugawira ena...Aheb 13:16[onaninso: dudukira, gawana]

GAWO (heritage)pakuti gawo lake ndi limeneli...Mlal 3:22pokhala gawo lake lenileni...Mlal 5:18[onaninso: cholowa, lanulanu]

GAWO (portion)pakuti gawo la Yehova...Deut 32:9mudzalandira chigawo...Yes 61:7

GAYO (Gaius)— mnzake wa Paulo...Mac 19:29)— wotembenuka mtima kumene wa ku Deribe...Mac 20:4— analandira Paulo ku Korinto...Aro 16:23;1Akor 1:14

GAZA (Gaza)mzinda wa Afilisti...Yos 13:3Samsoni anachotsa zipata zake...Ower 16:1-3)Samisoni anatengedwerako ngati wa m’ndende; kubwezerakwake...Ower 16:21-31tchimo lake linatsutsidwa...Amo 1:6,7maulendo a Filipo opita kumeneku...Mac 8:26

GEDALIYA (Gedaliah)anakhala kazembe Yuda...2 Maf 25:22-26anachita ubwenzi ndi Yeremiya...Yer 40:5,6anaphedwa ndi Ismaele...Yer 41:2,18

GEHAZI (Gehaz)kapolo wa Elisa; anafuna mphotho kuchokera kwa Naamani...2Maf 5:20-24azunzika ndi khate...2 Maf 5:25-27anafotokozera ntchito za Elisa kwa Yehoramu...2 Maf 8:4-6

GEHENA (hell)ku moto wa ku gehena...Mat 5:22ukaponyedwe kumoto wa gehena...Mat 18:9bwanji chilango cha ku gehena...Mat 23:33mphamvu za kumponya m’gehena...Luk 12:5moto wake ngochokera ku gehena...Yak 3:6[onaninso: dziko la anthu akufa]

GERARI (Gerar)mzinda wa Filisitiya...Gen 10:19unachezeredwa ndi Abrahamu...Gen 20:1-18unachezeredwa ndi Isake...Gen 26:1-17mfumu yake inali Abimeleki...Gen 26:1,26

GERESOMO (Gershom)mwana wamwamuna wa Mose...Eks 2:21-22unadulidwa...Eks 4:25amene anayambitsa banja la Alevi...1 Mbir 23:14-16

GESURI (Geshur)anthu ake sanachotsedwe ndi Israeli...Yos 13:13Talimai inali mfumu yake, agogo ake a Abisalomu...2 Sam 3:3Abisalomu anathawirako...2 Sam 13:37,38

GETSEMANI (Gethsemane)munda umene unali pafupi ndi Yerusalemu...Mat 26:30,36

Yesu amapitapitako...Luk 22:39kumalo omwe Khristu anamva zowawa ndikuperekedwa...Mat 26:36-56;Yoh 18:1-12

GEZERE (Gezer)mzinda wa Akanani...Yos 10:33anthu okhalamo sanachotsedwe...Yos 16:10anapatsidwa ngati lobola kwa mwana wamkazi wa Farao...1Maf 9:15-17

GIBEA (Gibeah)mzinda wa Benjamini, wodziwika ndi kuchita zoipa...Ower19:12-30unaonongedwa...Ower 20:1-48malo amene Saulo anabadwira...1 Sam 10:26mzida waukulu wa Saulo...1 Sam 15:34kuchita zoipa kwake, kunakumbukiridwa...Hos 9:9

GIBIYONI (Gibeon)malo amene dzuwa linaima chiliri...Yos 10:12malo omwe kunali hema...1 Mbir 16:39malo amene Yowabu anakantha Amasa...2 Sam 20:8-10malo amene Yowabu anaphedwera...1 Maf 2:28-34malo omwe Solomoni anaperekera nsembe komanso analotamaloto...1 Maf 3:5-15

GIDEONI (Gideon)anaitanidwa ndi m’ngelo...Ower 6:11-24anaphwanya guwa la nsembe la Baala...Ower 6:25-32ubweya unatsimikiza maitanidwe ochokera kwaMulungu...Ower 6:36-40anabwezera kwa Sukotiwo ndi Penuwele...Ower 8:4-21anakana ufumu, anapanga Efodi...Ower 8:22-28anakhala tate wa ana 71 kenaka anafa...Ower 8:29-35

GIHONI (Gihon)mtsinje wa mu Edeni...Gen 2:13— kasupe (chitsime) kunja kwa Yerusalemu...1 Maf 1:33-45gwelo la kochokera madzi...2 Mbir 32:30

GILIBOWA (Gilboa)mapiri otambalala a miyala yozilira (limestone) ku Isaka...1Sam 28:4malo omwe Saulo anafera...1 Sam 31:1-9anali pansi pa temberero la Davide...2 Sam 1:17, 21

GILIGALA (Gilgal)malo a miyala ya chikumbutso, mdulidwe komanso mgonero woyamba mdziko lamalonjezano...Yos 4:19-5:12malo a chipangano cha Agibeoni...Yos 9:3-15dera limodzi la malo omwe Saulo anayenda...1 Sam 7:15,16Saulo anakhala mfumu koma kenaka anakanidwa...1 Sam11:15;13:4-15linakanidwa chifukwa chopembedza mafano...Hos 9:15

GILIYADI (Gilead)chigwa kum’mawa kwa Yordane; chotengedwa kuchokera kwaAamori ndi kupatsidwa kwa Gadi, Rubeni ndi Manase...Num21:21-31;32:33-40;Deut 3:12,13;Yosw 13:24-31Isiboseti analamulira...2 Sam 2:8,9Davide anathawirako...2 Sam 17:21-26ogonjetsedwa ndi Hazaele...2 Maf 10:32,33mafuta ake okhala ndi machiritso...Yer 8:22

GOGI (Gog)kalonga wamkulu wa mzinda wa Meseki ndi wa Tubala...Ezek38:2,3— mtsogoleri wa nkhondo yotsiriza...Chiv 20:8-15

GOLI (yoke)udzachotsa goli lake pakhosi lake...Gen 27:40

Page 49: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

analemeretsa goli lathu…1 Maf 12:4senzani goli langa...Mat 11:29

GOLIDE (gold)golide wa kumeneko ndi wabwino...Gen 2:12uzipanga chotetezera cha golidi...Eks 25:17asadzichulutsire kwambiri siliva ndi golidi...Deut 17:17ngati ndayesa golidi chiyembekezo...Yob 31:24golidi wambiri woyengeka...Mas 19:10akunga zipatso za golidi...Miy 25:11siliva ndi wanga, golidi ndi wanga...Hagai 2:8siliva ndi golidi ndiribe...Mac 3:6ndi golidi kapena ngale...1 Tim 2:9munthu wovala mphete ya golidi...Yak 2:2golidi wanu ndi siliva wanu...Yak 5:3mtengo wake woposa wa golidi...1 Pet 1:7ndi zovunda, golidi ndi siliva...1 Pet 1:18la mzinda ndi la golidi...Chiv 21:21

GOLIYATI (Goliath)munthu wamphamvu wa ku Gati...1 Sam 17:4anaphedwa ndi Davide...1 Sam 17:50— mbale wake anaphedwa ndi Elihanani...2 Sam 21:19

GOLOGOTA (Golgotha)pamene Yesu anafera...Mat 27:33-35

GOMERI (Gomer)mwana wa Yafeti...Gen 10:2,3;1 Mbir 1:5,6— ufumu wa kum’mawa...Ezek 38:6— mkazi wake wa Hoseya...Hos 1:2,3

GOMORA (Gomorrah)ndi Sodomu, anagonjetsedwa ndi Kedorilaomere; Lotianatengedwa...Gen 14:8-12anaonongedwa ndi Mulungu...Gen 19:23-29watchulidwanso...Yes 1:10;Amosi 4:11;Mat 10:15

GONA (lying)mwana wokuta ndi nsalu atagona modyera...Luk 2:12[onaninso: bodza, khala, nama]

GONA (sleep)mukukhala ngati mwagona...Mas 44:23sadzaodzera kapena kugona...Mas 121:4ndi kukagona mochedwa...Mas 127:2iwo ajatu sangagone…Miy 4:16ndingogonako pang’ono...Miy 6:10bwanji mukugona...Luk 22:46monga mukugonabe...Mat 26:45Petro adaagona...Mac 12:6[onaninso: tulo]

GONA (sleeps)koma womangogona...Miy 10:5bwenzi lathu lagona...Yoh 11:11[onaninso: tulo]

GONA (slept)ndinagona tulo...Mas 3:5koma pamene anthu analinkugona...Mat 13:25

GONJETSA (conquer)ngati wogonjetsa kuchokera ku...Chiv 6:2

GONJETSA (overcome)gonjetsani choipa...Aro 12:21[onaninso: laka, pambana]

GONJETSA (possess)mbeu zako zidzagonjetsa...Gen 22:17[onaninso: khala, landira]

GONTHA (deaf)kapena wogontha...Eks 4:11makutu a ogontha adzatsegulidwa...Yes 35:5m’makutu mwawo mudzagontha...Mika 7:16[onaninso: gonthi, ogontha]

GONTHI (deaf)gonthi adamva mau a m’buku...Yes 29:18pena wagonthi monga mthenga wanga...Yes 42:19ali ndi maso, ndi agonthi...Yes 43:8[onaninso: gontha, ogontha]

GOSENI (Goshen)dera ku Ejipito komwe Aisraeli amakhala, malo abwino koposaGen 45:10;46:28,29;47:1-11

GRIKI (Greek)cha Aroma ndiponso cha Agriki...Yoh 19:20Tito, ngakhale ndi Mgriki...Agal 2:3[onaninso: Mhelene]

GUGUDA (beat)komatu anadziguguda pachifuwa...Luk 18:13[onaninso: menya, panda, puntha]

GULA (bought)m’dzanja lake la iye adachigulayo...Lev 25:28koma ndidzagula kwa iwe...2 Sam 24:24ndipo ndinagula mundawo...Yer 32:9naigula iwo...Mat 13:46munagulidwa ndi mtengo wake...1 Akor 6:20nadzakana Ambuye amene anawagula...2 Pet 2:1

GULA (buy)kudzagula tirigu...Gen 41:57gula ntheradi...Miy 23:23idzani mugule...Yes 55:1tigule osauka ndi...Amo 8:6gula zimene zitisowa...Yoh 13:29ndi iwo akugula...1 Akor 7:30ugule golidi kwa ine...Chiv 3:18munthu sangakhoza kugula...Chiv 13:17

GULA (buys)za munda, naugula...Miy 31:16nagula munda umenewu...Mat 13:44palibe munthu agulanso...Chiv 18:11

GULITSA (sell)mwagulitsa anthu anu...Mas 44:12anagulitsa anthu a chilungamo...Amo 2:6kagulitse zonse zimene uli nazo...Marko 10:21agulitse mwinjiro wake...Luk 22:36kugula kapena kugulitsa...Chiv 13:17nagulitsa ukulu wake...Gen 25:33pajatu atigulitsa...Est 7:4amakagulitsa zonse zimene...Mat 13:46ankagulitsa malonda...Luk 17:28ankagulitsa minda yao...Mac 2:45imene amagulitsa pamsika...1 Akor 10:25[onaninso: gulitsidwa]

GULITSIDWA (sell)imene idagulitsidwa mumzinda...Lev 25:33amene adagulitsidwa...Mas 105:17wogulitsidwa ngati kapolo...Aro 7:14[onaninso: gulitsa]

GULU LA AKULU AMPINGO (eldership)gulu la akulu ampingo lidakusanjika manja...1 Tim 4:14

Page 50: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

GULU LA NKHOSA (flock)anthu anu ngati gulu la nkhosa...Mas 77:20anawatsogolera ngati gulu la zoweta...Mas 78:52musaope, kagulu kankhosa inu...Luk 12:32[onaninso: gulu, nkhosa, zoweta]

GULU LA ANKHONDO (army)kukula kwa gulu lake la ankhondo...Mas 33:16gulu la ankhondo lalikulu ndithu...Ezek 37:10[onaninso: ankhondo]

GULU (band)ndi gulu la mbala...Hos 7:1[onaninso: lamba]

GULU (flock)osadya mkaka wake wa gululo...1 Akor 9:7wetani gulu la Mulungu...1 Pet 5:2okhala zitsanzo za gululo...1 Pet 5:3[onaninso:gulu la nkhosa, nkhosa, zoweta]

GUWA LA NSEMBE (altar)ndipo Nowa anamanga guwa la nsembe...Gen 8:20undiumbire guwa la nsembe...Eks 20:24nkhuni za pa guwa la nsembe...Lev 6:9ndakupatsa uwu pa guwa la nsembe...Lev 17:11chiperekere guwa la nsembe...Num 7:84analitcha guwa la nsembe...Yos 22:34nagumule guwa la nsembe...Ower 6:25mukamangire Yehova guwa la nsembe...2 Sam 24:18kutemberera guwa la nsembe...1 Maf 13:2kufikira guwa la nsembe...Mas 43:4padzakhala guwa la nsembe...Yes 19:19wataya guwa lake la nsembe...Mali 2:7mukuta guwa la nsembe la...Mal 2:13mtulo wako pa guwa la nsembe...Mat 5:23kutchula guwa la nsembe...Mat 23:18ndipezanso guwa la nsembe...Mac 17:23akuimirira guwa la nsembe...1 Akor 9:13alibe chiyanjano ndi guwa la nsembe...1 Akor 10:18tili nalo guwa la nsembe...Aheb 13:10nsembe pa guwa la nsembe...Yak 2:21anaima pa guwa la nsembe...Chiv 8:3

GWADA (bow)Usagwadira milungu yao...Eks 23:24kuitumikira ndi kuigwadira...Ower 2:19osagwadira Baala...1 Maf 19:18ndipo anagwada...Mat 27:29amene sanagwadira Baala...Aro 11:4[onaninso: uta, werama]

GWADIRA (worship)ndipo iwe umgwadire...Mas 45:11[onaninso: lambira, pembedza, pemphera]

GWETSA (cast)anthu akakugwetsa pansi...Yob 22:29ndipo mundigwetsa...Mas 102:10[onaninso: taya]

GWIDWA (hold)ndigwidwa mtima wosanena kanthu...Mas 77:4[onaninso: gwira, sunga]

GWIRA (catch)alalira kugwira wozunzika...Mas 10:9[onaninso: kola, sodza]

GWIRA (catches)iye agwira anzeru...1 Akor 3:19[onaninso: kwatula]

GWIRA (caught)yogwiridwa ndi nyanga zake...Gen 22:13sanagwira kanthu...Yoh 21:3[onaninso: kwatula, kwatulidwa]

GWIRA (cling)gwirizana nacho chabwino...Aro 12:9[onaninso: khudza, matirira]

GWIRA (hold)nilidzandigwira dzanja lanu...Mas 139:10ndidzagwira dzanja lako...Yes 41:13ngati mumgwiritsa monga momwe...1 Akor 15:2Mulungu, tigwiritse chikhulupiriro...Aheb 4:14[onaninso: gwidwa, sunga]

GWIRIZANA (consist)zonse zigwirizana pamodzi...Akol 1:17

GWIRIZANA (agree)umboni wawo sunkagwirizana...Marko 14:56[onaninso: vomerezana]

GWIRIZITSA (uphold)kapena kugwirizitsa ochita...Yob 8:20[onaninso: chirikiza, sankhula]

H

HABAKUKU (Habakkuk)mneneri wa Yuda, yuda asanagonjetsedwe ndi Babulo...Hab 1:1pemphero lake lotamanda Mulungu...Hab 3:1-19

HADASA (Hadassah)dzina la Estere la Chiyuda ...Est 2:7

HAGAI (Haggai)Mneneri nthawi ya Zekariya...Ezara 5:1,2;6:14;Hagai 1:1

HAGARA (Hagar)mdzakazi wake wa Sara, anaberekera Abrahamu Ismaele...Gen16Abrahamu anamthamangitsa; Mulungu anamutonthozaiye...Gen 21:9-21Paulo anafotokozera tanthauzo kuchokera ku zimenezi...Agal4:22-31

HAGITI (Haggith)m’modzi wa akazi a Davide...2 Sam 3:4Mayi ake a Adoniya...1 Maf 1:5

HAKOZI (Hakkoz)zidzukulu za Aaroni...1 Mbir 24:1,10anatchedwa Kozi...Ezara 2:61,62zidzukulu zake zinachotsedwa unsembe...Neh 7:63,64

HAMANI (Haman)anakonza chiwembu choononga a Yuda...Est 3:3-15anaitanidwa kuphwando lokonzedwa ndi Estere...Est 5:1-14anaumirizidwa kupatsa ulemu Moreidekai...Est 6:5-14anapachikidwa pa mtanda wake womwe...Est 7:1-10

HAMATI (Hamath)malire kum’mawa kwa Israel...Num 34:8;1 Maf 8:65;Ezek47:16-20anagonjetsedwa...2 Maf 18:34;Yer 49:23Aisraeli anakhala akapolo kumeneko...Yes 11:11

HAMORI (Hamor)anagulitsa malo kwa Yakobo...Gen 33:18-20;Mac 7:16anaphedwa ndi ana a Yakobo...Gen 34:1-31

Page 51: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

HAMU (Ham)mwana wamwamuna wochepetsetsa wa Nowa...Gen 5:32analowa mchombo...Gen 7:7khalidwe lake loipa linapangitsa Nowa kuti amtemberere...Gen9:22-25tate wa zidzukulu zake zomwe zinakhalapo dzikolinasanadzaze...Gen 10:6-20

HANA (Hannah)mkazi wosabereka wa Elikana; anapempherera mwana wamwamuna...1 Sam 1:1-18anabereka Samuele ndipo anampereka kwa Ambuye...1Sam1:19-28analemekeza Mulungu...1 Sam 2:1-10

HANANI (Hanani)atate aka a mneneri Yehu...1 Maf 16:1-7anadzudzula Asa, anaikidwa mndende...2 Mbir 16:7-10— mbale wake wa Nehemiya anabweretsa uthenga wokhudza aYuda...Neh 1:2anakhala bwanamkubwa wa Yerusalemu...Neh 7:2

HANANIYA (Hananiah)mneneri wonyenga amene ananena zotsutsana ndiYeremiya...Yer 28:1-17— dzina la chihebri la Sadreki...Dan 1:6,7,11

HANUNI (Hanun)mfumu ya Aamoni; anachititsa manyazi akazembe a Davide,anaphedwa ndi Davide...2 Sam 10:1-14

HARANI (Haran)mbale wa Abrahamu wamng’ono...Gen 11:26-31mzinda wa Mesepotamiya...Gen 11:31Abrahamu anachokako...Gen 12:4,5Yakobo anakhalako...Gen 29:4-35

HEBRONI (Hebron)Abramu...Isake, ndi Yakobo anakhala kumeneko...Gen13:18;23:2-20;35:27azondi anapitako...Num 13:21,22anagonjetsedwa ndi Yoswa...Yos 10:1-37cholowa cha Kalebi...Yos 14:12-15mzinda waukulu wa Davide; ana ake amuna anabadwakumeneko...2 Sam 2:1-3,11;3:2-5malo omwe Absalomu adaukira...2 Sam 15:7-10

HEMA (canopy)hema wa womzinga...Mas 18:11

HEMA (tent)udzapeza kuti pahema ...Yob 5:24monga hema wa mbusa...Yes 38:12kuza malo a hema wako...Yes 54:2hema wanga waonongeka...Yer 10:20[onaninso: msasa]

HEMANI (Heman)wolemba salimo, mutu wa Masalimo 88

HEREMONI (Hermon)phiri lalitali kwambiri (9,166 ft/mapazi) ku Siriya;

lotchedwansoSirioni, Seniri...Deut 3:8,9

HERMESI (Hermes)Paulo anayesedwa kukhala Hermesi...Mac 14:12

HERODE (Herod)— Herode wamkulu, wolamulira Yudeya (37-4BC)...Luk 1:5anafunsa za kubadwa kwa Yesu...Mat 2:3-8

anapha makanda a ku Betelehemu...Mat 2:12-18— Herode Antipa, wolamulira Galileya ndi Pereya (4BC-AD39)...Luk 3:1anaika m’ndende Yohane m’batizi...Luk 3:18-21anamdulitsa Yohane m’batizi mutu...Mat 14:1-12anasokonezeka chifukwa cha Yesu...Luk 9:7-9Yesu anatumizidwa kwa iye...Luk 23:7-11— Herode Agrippa woyamba (AD 37-44)...Mac 12:1,19anapha Yakobo...Mac 12:1,2anaika mndende Petro...Mac 12:3-11,19anaphedwa ndi mngelo...Mac 12:20-23— Herode Agripa wachiwiri (AD 53-70);wotchedwa Agripa komanso mfumu Agrippa...Mac25:22-24,26Festo anamuuza za Paulo...Mac 25:13-27Paulo analankhula moziteteza pamaso pake...Mac 26:1-32

HERODIYA (Herodias)chidzukulu chachikazi cha Herodi wotchuka; anakonza za imfaya Yohane...Mat 14:3-12anakwatiwa ndi amalume ake...Marko 6:17,18

HESIBONI (Heshbon)mzinda wakalekale wa Amoabu; wotengedwa ndi Mose...Num21:23-34unapatsidwa kwa Arubeni...Num 32:1-37mauneneri akhudza mzindawu...Yes 15:1-4;16:8-14;Yer48:2,34,35

HETI (Heth)mwana wa Kanani...Gen 10:15Abrahamu anagula munda kuchokera kwa ana ake...Gen23:3-20Esau anakwatira ana ake akazi...Gen 27:46

HEZEKIYA (Hezekiah)mfumu yolungama ya Yuda; anasintha mapembedzedwe amkachisi...2 Mbir 29-31anakangana/menyana ndi Asiriya; pemphero la chiombololinayankhidwa...2 Mbir 18:7-19:37kudwala kwake ndi kuchira kwake; chithokozo...2 Maf20:1-11;Yes 38:9-22anazikuza kwa Akazembe a ku Babiloni...2 Maf 20:12-19imfa yake...2 Maf. 20:20,21

HIDIKELI (Hiddekel)dzina la chihebri la mtsinje wa Tayigirisi...Gen 2:14;Dan 10:4

HILIKIYA (Hilkiah)mwana wa Salumu...1 Mbir 6:13wamkulu wansembe nthawi yaulamuliro wa Yosiya...2 Mbir34:9-22amayang’anira ntchito ya mkachisi...2 Maf 22:4-7anapeza buku la chilamulo...2 Maf. 22:8-14anathandiza za kusinthanso...2 Maf 23:4

HIMENEO (Hymenaeus)mphunzitsi wonyenga yemwe anachotsedwa ndi Paulo...1Tim 1:19,20

HINOMU, CHIGWA CHA MWANA WA (Hinom, valley of the sonof)

(onani TOPHET)malo pafupi ndi Yerusalemu,operekera nsembe za anthu ...2 Maf 23:10;2 Mbir 28:3;Yer7:31,32;19:1-5

HIRAMU (Hiram)mfumu ya ku Turoanam’mangira Davide nyumba ya chifumuanam’mangira Solomoni kachisi...2 Sam 5:11;1 Maf5:1-12;9:10-14,26-28;10:11;1 Mbir 14:1

Page 52: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

HISOPE (hyssop)mundiyeretse ndi hisope...Mas 51:7ku kamtengo ka hisope...Yoh 19:29

HIYELI (Hiel)Anthu a ku Beteli, anamanganso Yeriko...1 Maf 16:34anakwaniritsa temberero la Yoswa...Yos 6:26

HOFINI (Hophni)mwana woipa wa Eli...1 Sam 1:3;2:12-17,22-25uneneri wokhudzana naye...1 Sam 2:27-36;3:11-14ananyamula bokosi la chipangano kupita nalo ku nkhondo;anakaphedwa...1 Sam 4:1-11

HOREBU (Horeb)(onani SINAI)Mulungu anaonekera kwa Mose pamenepo...Eks 3:1-22madzi anatsika kuchokera...Eks 17:6Eliya anakhalako masiku 40...1 Maf 19:8,9

HORO (Hor)phiri la ku Edomu; malo aimfa ya Aaroni...Num20:22-29;33:37-39

HOSEYA (Hosea)mwana wa Beeri; mneneri wa ufumu wa kum’mawa...Hos 1:1

HOSEYA (Hoshea)dzina lenileni la Yoswa mwana wa Nuni...Deut 32:44;Num13:8,16— mfumu yomaliza ya Israeli, inalanda ufumu mwaupandu...2

Maf 15:30inalamulira moipa;Israeli anatengedwa ukapolo kupita ku Asiriya nthawi ya

ulamuliro wake...2 Maf 17:1-23

HULIDA (Hulda)mkazi wa Salumu...2 Maf 22:14analosera za kugwa kwa Yerusalemu...2 Maf 22:15-17;2 Mbir34:22-25anaipulumutsa mfumu ku mavuto omwe idakaona...2 Maf

22:18-20

HURAMU (Huram)mkulu waluso popanga zinthu za mkuwa...1 Maf 7:13-40,45;2

Mbir 2:13,14

HURI (Hur)munthu wa ku Yuda; wa mnyumba ya Kalebu...1 Mbir 2:18-20anathandizira manja a Mose...Eks 17:10-12anathandiza Aaroni...Eks 24:14

HUSAI (Hushai)mlaliki; mnzake wa Davide...2 Sam 15:32-37ananamizira kumvera chisoni Absalomu...2 Sam 16:16-19anagonjetsa malangizo a Ahitofele...2 Sam 17:5-23

IIBA (steal)

mphawi usamubere...Miy 22:22ntchito yake nkuba...Ezek 18:10usabe...Eks 20:15mumaba mumapha...Yer 7:9aneneri amene amaberana...Yer 23:30mbala zimathyola ndi kuba...Mat 6:19angadzabwere kudzaba...Mat 27:64usachite chigololo, usabe...Marko 10:19amangodzera kuba...Yoh 10:10wolalika kuti osamaba...Aro 2:21amene ankaba...Aef 4:28

IBIZANI (Ibzan)oweruza wa Israeli, tate wa ana 60...Ower 12:8,9

IDA (dark)wakuda ine koma wokongola...Nyi 1:5nasanduliza usana kuti ude ngati usiku...Amo 5:8ndi usana udzawadera...Mik 3:6[onaninso: mdima]

IDA (darkened)dziko lonse kuti dziko linada...Eks 10:15m’maso mwao mude...Mas 69:23[onaninso: detsedwa]

IDA NKHAWA (despaired)kotero kuti tinada nkhawa...2 Akor 1:8[onaninso: khululuka]

IDO (Iddo)wamkulu wa Ayuda a ku Kasifiya...Ezara 8:17-20woonerera masomphenya amene zolemba zake zinaonedwa...2Mbir 9:29

IDYA (devour)chitemberero chadya...Yes 24:6lupanga lanu ladya...Yer 2:30[onaninso: dyana, dyera, likwira]

IDYA (dine)adamuitana kuti akadye naye...Luk 11:37ndipo ndidzadya naye...Chiv 3:20

IDZA (comes)ndani uyu ali nkudza...Yes 63:1ndi kwa wina idza, nadza...Mat 8:9kufikira akadza iye...1 Akor 11:26[onaninso: fika]

IDZA (coming)likudza tsiku lotentha...Mal 4:1koma iye wakudza pambuyo panga...Mat 3:11inu ndinu wakudza kodi...Mat 11:3alinkudza m’mitambo...Marko 13:26wakundiposa ine mphamvu alinkudza...Luk 3:16lonjezano lakudza kwake...2 Pet 3:4ndidza msanga, gwira chimene uli nacho...Chiv 3:11ndipo taonani, ndidza msanga...Chiv 22:7anena, indetu ndidza msanga...Chiv 22:20

IFA (die)ukadzadya, ndithu udzafa...Gen 2:17munthu aliyense adzafera...2 Mbir 25:4anthu anzeru amafa...Mas 49:10sindidzafa...Mas 118:17m’menemonso amafera munthu wanzeru...Mlal 2:16nanga uferenji nthawi...Mlal 7:17adzafa ali wochimwa...Ezek 3:19ngakhale ine ndikafa...Mat 26:35mwakuti sangafenso ai...Luk 20:36munthu akachidya asafe...Yoh 6:50ndakuuzani kuti mudzafera...Yoh 8:24ngakhale afe adzakhala ...Yoh 11:25kuti munthu m’modzi afere anthu...Yoh 11:50Yesu adzafera mtunduwo...Yoh 11:51Yesu adzafera mtundu...Yoh 19:7mutsata khalidwelo, mudzafa...Aro 8:13kufa kuli kupindula...Afil 1:21kwa anthu kufa kamodzi...Aheb 9:27[onaninso: mwalira]

IFA (died)ndipo zinafa zamoyo zonse...Gen 7:21

Page 53: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

Ha! bwenzi titafa...Eks 16:3Khristu adatifera ife...Aro 5:6ochimwabe, Khristu adatifera...Aro 5:8pakuti munthu akafa...Aro 6:7ngati tidafa pamodzi...Aro 6:8ndipo ine ndinafa...Aro 7:9m’modzi adafera onse...2 Akor 5:14iye adafera anthu onse...2 Akor 5:15mwa lamulo ndafa...Agal 2:19adatifera kuti tikakhale ndi moyo...1 Ates 5:10ngati tidafa pamodzi naye...2 Tim 2:11chikhulupiriro chawo mpaka kufa...Aheb 11:13m’machimo tikhale ngati akufa...1 Pet 2:24[onaninso: mwalira]

IFA (dies)itapanda kufa...1 Akor 15:36

IKA (appoint)ndidzakuikirani zoopsa...Lev 26:16nimuikire munthu aliyense...Num 4:19adzaika chipulumutso chikhale...Yes 26:1sanatiika ife tilawe mkwiyo...1 Ates 5:9nukaike akulu m’midzi...Tit 1:5[onaninso: sankha]

IKA (appointed)popeza kwaikikatu...Aheb 9:27[onaninso: lembedwa, yenera]

IKA (bury)muike wakufa wanu m’manda...Gen 23:6panalibe wakuwaika...Mas 79:3kuika maliro...Mat 8:21akufa aike akufa...Mat 8:22

IKA (lay)aliyense ndiikapo manja...Mac 8:19usafulumira kuika manja...1 Tim 5:22[onaninso: samira, vula]

IKA M’MANDA (burial)pa kuikidwa kwanga...Mat 26:12tsiku lakuikidwa kwanga...Yoh 12:7anamuika Stefano...Mac 8:2[onaninso: maliro]

IKABODI (Ichabod)mwana wa Finehasi...1 Sam 4:19-22

IKIDWA M’MANDA (buried)ndi kuikidwa komweko...Rut 1:17ndinaona oipa alikuikidwa...Mlal 8:10natola mtembo, nauika...Mat 14:12naikidwa m’manda...Luk 16:22tinaikidwa m’manda...Aro 6:4ndi kuti anaikidwa m’manda...1 Akor 15:4popeza munaikidwa m’manda...Akol 2:12

IKONIO (Iconium)mzinda wa ku Asiya wamng’ono...Mac 13:51kumene wotembenuka mtima anali...Mac 14:1-6

IMA (conceive)taonani namwali adzaima...Yes 7:14[onaninso: khala ndi pakati]

IMA (conceived)pamenepo chilakolako chitaima...Yak 1:15[onaninso: badwa, pathupi]

IMA (stand)

palibe munthu m’modzi adzaima pamaso panu...Deut7:24

akhoza ndani kuima pamaso pa Mulungu...1 Sam 6:20oipa sadzaimirira pa mlanduwo...Mas 1:5muimiranji patali Yehova...Mas 10:1nadzaima m’malo ake oyera ndani...Mas 24:3ndi mdani aime pa dzanja lamanja lake...Mas 109:6adzaima pamaso pa mafumu...Miy 22:29usaumirire kanthu koipa...Mlal 8:3upo wao sudzaima ai...Yes 7:7imani m’njira ndi kuona, funsani...Yer 6:16sadzasowa munthu wakuima pamaso panga...Yer 35:19adzaima ndani pa kulunda kwake...Nah 1:6ndipo adzaima ndani pooneka Iye...Malak 3:2Iye aimirira kapena kugwa kwa mbuye wake...Aro 14:4pakuti ndi chikhulupiriro muimadi...2 Akor 1:24kuti mudzakhoza kuima chitsutsire...Aef 6:13m’chimenechi muimemo...1 Pet 5:12taona ndaima pakhomo...Chiv 3:20[onaninso: chirimika, khala, khazikika, limba, tsimikizidwa,

uka]IMBA (sing)

imbirani Chauta...Eks 15:21imbani nyimbo zoyamika...Mas 66:2ndidzaimba nyimbo...Mas 101:1kuti tiimbe nyimbo...Mas 137:3tatiimbiraniko nyimbo...Mas 137:3adzaimba mokondwa...Yes 65:14ndidzaimba ndi mtima...1 Akor 14:15aimbe nyimbo zotamanda...Yak 5:13nthawi yoimba...Nyi 2:12muziimbira Ambuye...Aef 5:19

IMFA (death)inu ndi ine, koma imfa ndiyo...Rut 1:17dziko la mdima ndi lamthunzi wa imfa...Yob 10:21ndidziwa kuti mudzandifikitsa ku imfa...Yob 30:23pakuti muimfa m’mosakumbukira inu...Mas 6:5kuti ndingagone tulo taimfa...Mas 13:3ndingakhalele ndiyende mchigwa cha mthunzi wa imfa...Mas23:4mwalandira moyo wanga kuimfa...Mas 56:13adzakhalabe ndi moyo, osaona imfa...Mas 89:48nyumba yake itsikira kuimfa...Miy 2:18onse akundida ine akonda imfa...Miy 8:36lilime liri ndi mphamvu pa imfa...Miy 18:21iye wameza imfa kunthawi yonse...Yes 25:8pakuti sindikondwera nayo imfa...Ezek 18:32ndidzawaombola ku imfa...Hos 13:14sadzalawa ndithu imfa...Mat 16:28koma wachokera ku imfa...Yoh 5:24sadzaona imfa nthawi zonse...Yoh 8:51imfa inachita ufumu...Aro 5:14monga uchimo unachita ufumu mu imfa...Aro 5:21imfa siichitanso ufumu pa iye...Aro 6:9mphoto yake ya uchimo ndi imfa...Aro 6:23kuti zibalire imfa zipatso...Aro 7:5mulalikira imfa ya Ambuye...1 Akor 11:26monga imfa inadza mwa munthu...1 Akor 15:21cha imfa ichi chidzavala chosafa...1 Akor 15:54koma mbola ya imfa ndiyo uchimo...1 Akor 15:56kwa ena fungo la imfa...2 Akor 2:16imfa ichita mwa ife ...2 Akor 4:12chisoni chadziko lapansi chichita imfa...2 Akor 7:10nakhala omvera kufikira imfa...Afil 2:8alawe imfa m’malo mwa munthu...Aheb 2:9amene anali nayo mphamvu ya imfa...Aheb 2:14anatengedwa kuti angaone imfa...Aheb 11:5uchimo utakula msinkhu ubala imfa...Yak 1:15losati lakuimfa...1 Yoh 5:16khala wokhulupirika kufikira imfa...Chiv 2:10pa iwowa imfa yachiwiri ilibe...Chiv 20:6

Page 54: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

sipadzakhalanso imfa...Chiv 21:4ndiyo imfa yachiwiri...Chiv 21:8

IMVA (attend)imvani kupempha kwanga...Mas 17:1kuti mumve pemphero langa...Mas 86:6[onaninso: senza]

IMVA (attentive)Ambuye imvani liu langa...Mas 130:2anamlendewera Iye kuti amve...Luk 19:48

IMVI (gray)ndi chisoni imvi zanga kumanda...Gen 42:38pamodzi ndi munthu wa imvi...Deut 32:25kukongola kwa nkhalamba ndi imvi...Miy 20:29

IMVI (hair)imvi zomwe zampakiza osachidziwa...Hos 7:9[onaninso: tsitsi]

IMWA (drank)naamwa onse...Marko 14:23onse ankamwanso chakumwa...1 Akor 10:4

IMWA (drink)kodi ife timwa chiyani...Eks 15:24usamwe vinyo kapena chakumwa...Lev 10:9namwe mkwiyo wa wamphamvu yonse...Yob 21:20vinyo wosasa kuti ndimwe...Mas 69:21iwe uzimwera m’chitsime...Miy 5:15omwa zaukali amautsa...Miy 20:1kuti angamwe, naiwala...Miy 31:5udzimwa vinyo wako mosangalala...Mlal 9:7atumiki anga adzamwa...Yes 65:13bwerani nacho, timwe...Amo 4:1sindidzamwanso chakumwa cha...Mat 26:29wosanganiza ndi ndulu kuti amwe...Mat 27:34wosanganiza ndi mule kuti amwe...Marko 15:23mundipatseko madzi akumwa...Yoh 4:7abwere kwa ine kuti adzamwe...Yoh 7:37kumwa vinyo...Aro 14:21nthawi zonse mukamamwa...1 Akor 11:25uleke kumangomwa madzi okha...1Tim 5:23ankamwetsa anthu amitundu...Chiv 14:8[onaninso: chakumwa]

IMWA (drinks)munthu aliyense womwako madzi awa...Yoh 4:13ndi kumwa magazi anga...Yoh 6:54ndi kumwa chikho chimenechi...1 Akor 11:29[onaninso: zakumwa]

IMWA (drunk)ndikumwa vinyo wanga ndi...Nyi 5:1ndipo anthu atamwatu...Yoh 2:10

IPA (bad)kunena ndi iwe choipa kapena...Gen 24:50kapena yoipa m’malo mwa...Lev 27:10upatsa zipatso zoipa...Mat 7:17

IPA (wickedness)yodzaza ndi maganizo oipa...Gen 6:5kuipa kwao nkwakukulu...Yob 22:5m’nyumba za anthu oipa...Mas 84:10[onaninso: choipa, zoipa]

IPHA (murder)usaphe...Eks 20:13adawalamula kuti usaphe...Mat 5:21a Ambuye nkumafuna kuwapha...Mac 9:1

chake kumapha munthu...Yak 4:2za anthu amene adapha...Mat 23:31iye amene inu mudamupha...Mac 5:30ndipo adapha mbale wake...1 Yoh 3:12chikhaire ngwopha anthu...Yoh 8:44chifukwa choti wapha munthu...1 Pet 4:15aliyense wopha anthu...1Yoh 3:15wadzadza ndi anthu opha...Yes 1:21monga anthu opha atate ao...1Tim 1:9zonyansa, opha anzao ...Chiv 21:8

IPHA (murders)maganizo oipa, zakuphana...Mat 15:19

IPHWA (dried)kasupe wa nthenda yake adaphwa...Marko 5:29pomwepo madzi ake adaphwa...Chiv 16:12[onaninso: uma]

IPIDWA (abhor)ndipo sindidzaipidwa nanu...Lev 26:11mitundu ya anthu idzaipidwa naye...Miy 24:24[onaninso: dana, nyansa, nyansidwa]

IPIRA (displeased)zimene adachita Davidezi zidamuipira...2 Sam 11:27[onaninso: kwiya]

IPITSA (defile)ndizo ziipitsa munthu...Mat 15:18[onaninso: detsa]

IPITSA (defiled)ngakhale ndi chovala chao chomwe choipitsidwa ndimachimo...Yuda 23adawaipitsa powagwetsera pansi...Mas 74:7[onaninso: detsedwa]

IPITSA (defiles)chilowa mkamwa sichiipitsa...Mat 15:11

IPSA MTIMA (aroused)Chauta adapsa mtima...Num 11:10adapsa mtima Yobu...Yob 32:2[onaninso: dzuka]

IPSA (burn)chitsambacho sichilikupsa...Eks 3:3[onaninso: tentha]

ISAKI (Isaac)mwana wolonjezedwa wotenga cholowa cha pangano...Gen17:16-21anabadwa ndi kudulidwa...Gen 21:1-7anaperekedwa monga nsembe...Gen 22:1-19anakwatira Rabeka...Gen 24:62-67anapempherera ana, anakonda Esau...Gen 25:21-28zochita zake ndi Abimeleki; mfumu ya ku Gerani...Gen 26:1-31mosazindikira anamdalitsa Yakobo...Gen 27:1-28anafa muukalamba wake...Gen 35:28,29amatchulidwa mu chipangano chatsopano...Luk 3:34;Agal4:21-31;Aheb11:9,20

ISANU (five)adatola miyala isanu...1 Sam 17:40monga zikwi zisanu...Mat 14:21ndipo asanu anali opusa...Mat 25:2[onaninso: asanu, zisanu]

ISIBOSETI (Ishbosheth)m’modzi mwa ana a Saulo; anakhala mfumu...2 Sam 2:8-10anampweteketsa mtima Abineri...2 Sam 3:7-11anazingidwa, anthu omzingao anaphedwa monga mwa

Page 55: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

lamulo...2 Sam 4:1-12

ISKARIOTE, YUDASI (Iscariot, Judas)anali mgulu la khumi ndi awiri...Marko 3:14,19;Luk 6:16anamnena Maria...Yoh 12:3-6wodziwidwa kukhala wompereka Yesu...Yoh 13:21-30anatenga ndalama kuti ampereke Yesu...Mat 26:14-16anampereka Yesu pakumpsopsona...Marko 14:43-45analapa ndi kudzipha...Mat 27:3-10malo ake anaikidwapo munthu wina...Mac 1:15-26

ISMAELE (Ishmael)mwana wa Abrahamu kudzera mwa Hagara...Gen 16:3,4,11-16anadulidwa...Gen 17:25ananyodola anthu pa phwando la Isaki; anapititsidwa kuukapolo ndi mai ake...Gen 21:8-21ana ake; imfa yake...Gen 25:12-18mwana wa Netaniya; anapha Gedaliya...2 Maf 25:22-26

ISRAELI (Israel)motero dzina lako lidzakhala Israeli...Gen 32:28Imvani Israeli...Deut 6:4limodzi ndi ana onse a Israeli...2 Sam 7:7Indedi Mulungu achitira Israeli...Mas 73:1anathangatira Israeli mnyamata...Luk 1:54onse akuchokera kwa Israeli siali Israeli...Aro 9:6zikhale pa iwo ndi pa Israeli...Agal 6:16

ISRAELI (Israel)amagwiritsidwa ntchito kukhala:Yakobo...Gen 32:28zidzukulu za Yakobo...Gen 49:16,28mafuko khumi a kum’mawa (molekanitsa ndiYuda)...1 Sam11:8dziko lobwezeretsedwanso utatha ukapolo...Ezara 9:1mpingo weniweni...Agal 6:16

ISWA (broke)nawaswa m’tsinde mwa phiri...Eks 32:19pangano limene analiswa...Yer 31:32naswa nsupayo...Marko 14:3[onaninso: nyema]

ITANA (call)ndidzaitana kwa Yehova...1 Sam 12:17ndikuitanani, amuna...Miy 8:4itanani iye pamene ali pafupi...Yes 55:6undiitane ine, ndipo...Yer 33:3ukaitana Mulungu wako...Yon 1:6adzaitana dzina langa...Zek 13:9sindinadza kudzaitana olungama...Mat 9:13Ambuye Mulungu wathu adzaitana...Mac 2:39iwo adzaitana bwanji pa iye...Aro 10:14Mulungu sanaitana ife...1 Ates 4:7kukhazikitsa maitanidwe...2 Pet 1:10[onaninso: itcha]

ITANA (called)Ine Yehova ndakuitana iwe...Yes 42:6Yehova anandiitana ine ndisanabadwe...Yes 49:1ndinaitana mwana wanga...Hos 11:1ndinaitana mwana wanga aturuke...Mat 2:15Mulungu watiitana ife mumtendere...1 Akor 7:15amene anakuitanani muturuke...1 Pet 2:9Iye amene adatiitana ife...2 Pet 1:3[onaninso: itanidwa, itcha, tchedwa]

ITANA (calls)Ine Yehova ndakuitana...Yes 42:6Yehova anandiitana ine...Yes 49:1palibe amene aitana...Yes 64:7ndinaitana mwana wanga ali...Hos 11:1

mphatso zake ndi kuitana...Aro 11:29ndinaitana mwana wanga...Mat 2:15aitana nkhosa...Yoh 10:3ndiwo amene aitanidwa...Aro 8:30adzaitana pa dzina la Ambuye...Aro 10:13Mulungu waitana ife mumtendere...1 Akor 7:15za iye amene anakuitanani...1 Pet 2:9chidziwitso cha iye amene anatiitana ife...2 Pet 1:3[onaninso: itcha]

ITANIDWA (called)ndiwo amene aitanidwa...Aro 8:28[onaninso: itana, itcha, tchedwa]

ITCHA (call)atchapo dzina lawo...Mas 49:11adzamutcha dzina lake Yesu...Mat 1:21ndidzawatcha anthu anga...Aro 9:25[onaninso: itana]

ITCHA (called)ndipo Mulungu anatcha...Gen 1:5anamutcha dzina lake mkazi...Gen 3:20[onaninso: itana, itanidwa, tchedwa]

ITCHA (calls)adzitcha maina zonsezi...Mas 147:4atchula iye Ambuye...Marko 12:37[onaninso: itana]

ITHA (consume)ndingathe inu panjira...Eks 33:3moto waukuru uwu udzatitha...Deut 5:25muwathe mumkwiyo...Mas 59:13Ambuye Yesu adzamthera...2 Ates 2:8

ITHA (consumed)chifukwa chakusathedwa ife...Mali 3:22[onaninso: nyeka, ononga, tentha]

ITHA (end)zimenezi zidzatha bwanji...Dan 12:8nkutha kwake kwa dziko...Mat 13:39mpaka kutha kwa dziko lino...Mat 28:20kamodzi kokha pakutha...Aheb 9:26[onaninso: chimaliziro,chitsiriziro, maliza, mathero,

matsiriziro,tsiriza]

ITHA (finished)adati, “kwatha...Yoh 19:30mpaka zitatha zaka chikwi...Chiv 20:3

IWALA (forget)Mulungu wandiiwalitsa kusauka...Gen 41:51musaiwale chipangano chimene...Deut 4:23ndi makolo anu, sadzachiiwala...Deut 4:31musadzaiwale Chauta...Deut 6:12zimawachitikira anthu oiwala...Yob 8:13onse akuiwala Mulungu...Mas 9:17ichi inu oiwala Mulungu...Mas 50:22osaiwala zochita Mulungu...Mas 78:7sindidzaiwala mau anu...Mas 119:16ndikakuiwalani, Yerusalemu...Mas 137:5mwana wanga usaiwale...Miy 3:1mkazi angathe kuiwala mwana...Yes 49:15angakhale aiwale mwana wake...Yes 49:15ndinu yani kuti muziiwala Chauta...Yes 51:13namwali amaiwala zokongoletsa...Yer 2:32

IWALA (forgets)kuyiwala chipangano...Miy 2 :17

Page 56: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

nkuiwala m’mene akuonekera...Yak 1:24

IWALA (forgetting)ndimaiwala zakumbuyo...Afil 3:13

IWALA (forgot)Yosefe, koma anamuiwala...Gen 40:23naiwala Yehova Mulungu wao...Ower 3:7ndipo anaiwala zochita iye...Mas 78:11anaiwala ntchito zake msanga...Mas 106:13

IWALA (forgotten)mwaiwala Mulungu amene...Deut 32:18mwandiiwala chifukwa ninji...Mas 42:9tikadaiwala dzina la Mulungu...Mas 44:20pakuti angoiwalika,... Mlal 9:5Israeli, sindidzakuiwala...Yes 44:21Ambuye mwandiiwala ine...Yes 49:14mtendere ndinaiwala zabwino...Mali 3:17palibe imodzi ya izo iiwalika...Luk 12:6mwaiwala dandauliro limene...Aheb 12:5woiwala matsukidwe ake...2 Pet 1:9

K

KADUKA (envy)pamene pali kaduka ndi...Yak 3:16kaduka ndi masinjiriro onse...1 Pet 2:1onaninso: njiru, nsanje]

KAINI (Cain)mwana wamwamuna woyamba wa Adamu...Gen 4:1nsembe yake inakanidwa...Gen 4:2-7;Aheb 11:4anapha Abele; anakhala mdziko laweni, anakakhala kuNodi...Gen 4:8-17mtundu wa choipa...Yuda 11

KAISARA (Caesar)— Kaisara Augusto (31BC-A.D.14) lamulo lake linabweretsa Yosefe ndi Mariya ku

Betelehemu...Luk2:1— Tiberiyo Kaisara (A.D. 14-37), anakhalapo nthawi ya

utumikiwa Yesu...Luk 3:1-23msonkho umaperekedwa kwa iye...Mat 22:17-21Ayuda anakhala mbali yake...Yoh 19:12— Klaudiyo Kaisara (A.D. 41-54) kunali njala nthawi yaulamuliro wake...Mac 11:28anawaletsa Ayuda ku Roma...Mac 18:2— Nero Kaisara (A.D. 54-68) Paulo anaonekera kwa

iye...Mac25:8-12Akhristu anasinthikira mnyumba yake...Afil 4:22Paulo anayimbidwa mlandu koyambirira...2 Tim 4:16-18wotchedwa Augusto...Mac 25:21

KAISAREYA WA FILIPI (Caesarea Philippi)mzinda kumpoto kwa Palestinamalo amene Petro anavomereza kuti Yesu ndi Mesiya...Mat16:13-20akhozanso kukhala malo a masandulidwe a Yesu...Mat 17:1-3

KAISAREYA (Caesarea)mzinda waukulu wa chiroma ku Palestina...Mac 12:19;23:33Paulo anaperekezedwako...Mac 23:23-33kumene Paulo anamangidwaanafuna mlandu wake kuti ukakhale kubwalo lalikulu kwaKaisara...Mac 25:4,8-13Petro analalikirako...Mac 10:34-43Paulo analalikirako...Mac 9:26-30;18:22;21:8

KAKAMIZA (compel)

amene adakukakamizani kumperekeza...Mat 5:41[onaninso: umiriza]

KAKAMIZA (compels)amene adakukakamiza...Mat 5:41chikondi cha Khristu chitikakamiza...2 Akor 5:14[onaninso: fulumiza]

KAKOMBO (lily)ngati kakombo wa m’zigwa...Nyi 2:1muja amakhalira kakombo...Nyi 2:2adzachita maluwa ngati kakombo...Hos 14:5

KALAMBA (age)Abrahamu ndi Sara anali okalamba...Gen 18:11anali akhungu muukalamba...Gen 48:10kumanda utakalamba...Yob 5:26kwa okalamba kuli...Yob 12:12Paulo nkhalamba...Fil 9[onaninso: msinkhu, zaka]

KALATA (epistle)kalata yochitira umboniyo ndinu...2 Akor 3:2kuti ndinu kalata yochokera...2 Akor 3:3mau apakamwa kapena am’makalata...2 Ates 2:15talemba m’kalatayi...2 Ates 3:14chizindikiro changa m’kalata...2 Ates 3:17

KALAUDIASI LISIASI (Claudius Lysias)kapitawo wamkuru yemwe anamteteza Paulo...Mac24:22-24,26

KALDAYO (Chaldea)poyambirira anali mbali ya kumadzulo kwa Babulo...Gen 11:31kenaka anapatsidwa kwa Babulo yense...Dan 3:8nkumene Abramu anachokera...Gen 11:28-31

KALEBI (Caleb)anatumizidwa ngati mzondi, anapereka nkhani yabwinoyokhudza dziko lomwe anakazondaanapatsidwa mphotho...Num 13:2,6,27,30;14:5-9,24-38anapatsidwa Hebroni...Yos 14:6-15anagonjetsa mzinda wake pothandizidwa ndi Otiniyeli...Yos15:13-19

KALEKALE (ancient)malire akalekale...Miy 23:10ndidazikonzeratu kalekale...Yes 37:26nkhalamba ya kale lomwe...Dan 7:22

KALONGA (prince)iri kuti nyumba ya kalonga...Yob 21:28popanda anthu kalonga aonongeka...Miy 14:28kalonga wa mtendere...Yes 9:6wodzodzedwayo ndiye kalonga...Dan 9:25koma Mikaeli kalonga wanu...Dan 10:21opanda mfumu ndi opanda kalonga...Hos 3:4kalonga apempha ndi oweruza...Mika 7:3[onaninso: mkulu, mtsogoleri]

KANIZA (abstain)muzikanize...1 Pet 2:11[onaninso: letsa, lewa, pewa]

KAVALE (calvary)pamene Yesu anapachikidwa...Luk 23:33chimodzimodzinso “Golgota” mu Chihebri... Yoh 19:17

KAMA (bed)pokumbukira Inu pa kama wanga...Mas 63:6pakuti kama wafupika...Yes 28:20adzakhala awiri pa kama m’modzi...Luk 17:34

Page 57: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: mphasa, pogona, tchika]

KAMODZI (once)adafa kamodzi, kokhako...Aro 6:10aliyense amafa kamodzi...Aheb 9:27machimo a anthu kamodzi...1 Pet 3:18

KAMVULUVULU (whirlwind)Yobu mkamvuluvulu...Yob 38:1adakwera kumwamba mkavuluvulu...2 Maf 2:1

KANA (Cana)mudzi kum’mawa kwa Galileya; kwawo kwa Nataniyeli... Yoh21:2malo omwe chozizwa choyamba cha Yesu chinachitikira... Yoh2:1-11Yesu anachiritsapo munthu...Yoh 4:46-54

KANA (denied)pamenepo Petro anakananso...Yoh 18:27popeza tsono izi sitikanika...Mac 19:36wakana chikhulupiriro iye...1 Tim 5:8osakana dzina langa...Chiv 3:8[onaninso: kanidwa, kaniza]

KANA (denies)yense amene adzandikana...Mat 10:33wokanayo kuti Yesu sali Khristu...1 Yoh 2:22

KANA (deny)ndikhute ndi kukukanani...Miy 30:9pambuyo panga, adzikane yekha...Mat 16:24pakuti sakhoza kudzikana yekha...2 Tim 2:13ndi ntchito zao amkana iye...Tit 1:16nakaniza mfumu wayekha...Yuda 4osakaniza chikhulupiriro...Chiv 2:13

KANA (denying)mphamvu yake adaikana...2 Tim 3:5pokana chisapembedzo...Tit 2:12nadzakana Ambuye...2 Pet 2:1

KANA (rejected)mwala umene omangawo anaukana...Mas 118:22mwala umene anaukana omanga nyumba...Mat 21:42Mose uyu amene anamkana...Mac 7:35mwala umene omangawo anaukana...1 Pet 2:7[onaninso: kanidwa, kanizidwa, taya]

KANA (rejects)iye wakukana inu andikana Ine...Luk 10:16[onaninso: taya]

KANANI (Canaan)mwana wamwamuna wa Hamu...Gen 10:6anatembereredwa ndi Nowa...Gen 9:20-25— dziko la malonjezano...Gen 12:5malire a Kanani...Gen 10:19wokhudza malonjezano a Mulungu, anapatsidwa kwaAbrahamu...Gen 12:1-3anapatsidwa kwa Isake...Gen 26:2,3anapatsidwa kwa Yakobo...Gen 28:10-13anapatsidwa kwa Israeli...Eks 3:8kugonjetsa kwake kunaneneredweratu...Gen 15:7-21kunatsatidwa ndi ulendo wokazonda dzikoli...Num 13:1-33anachedwetsedwa kutenga dzikoli chifukwachosakhulupirira...Num 14:1-35chinakwaniritsidwa ndi Ambuye...Yos 23:1-16anakwaniritsidwa mbali imodzi yokha...Ower 1:21,27-36

KANGAMIRA (clings)

lilime langa likangamira ku nsaya...Mas 22:15[onaninso: matirira]

KANGAMIRA (covetousness)mtima wanu usakangamire pa ndalama...Aheb 13:5[onaninso: chisiriro, sirira, msiriro]

KANGANA (contend)ndidzakangana naye amene...Yes 49:25[onaninso: limbana, tsutsana]

KANIDWA (denied)adzakanidwa pamaso pa angelo...Luk 12:9pamenepo Petro anakananso...Yoh 18:27inu munakaniza woyera...Mac 3:14popeza tsono izi sitikanika...Mac 19:36wakana chikhulupiriro iye...1 Tim 5:8osakana dzina langa...Chiv 3:8[onaninso: kana, kaniza]

KANIDWA (rejected)iye ananyozedwa ndi kukanidwa...Yes 53:3mwala wamoyo wokanidwatu...1 Pet 2:4[onaninso: kana, kanizidwa, taya]

KANIZA (denied)inu munakaniza woyera...Mac 3:14[onaninso: kana, kanidwa]

KANIZA (reject)bwino mukaniza lamulo la Mulungu...Marko 7:9kamodzi ndi kawiri umkanize...Tit 3:10[onaninso: pepula, nyoza]

KANIZIDWA (rejected)nakanizidwe ndi mbadwo...Luk 17:25[onaninso: kana, kanidwa, taya]

KANJEZA (palm)pa nsanamilazo panali akanjedza...Ezek 40:16zidundumwa zake ndi akanjeza ake...Ezek 40:22chakuno ndi chauko panali akanjeza...Ezek 40:31nsanamira zake panali akanjeza...Ezek 40:34nsanamira zake panali akanjeza...Ezek 40:37anatenga makwata a kanjeza...Yoh 12:13

KANTHA (stricken)kumkantha ndi kunsautsa...Yes 53:4mumawakantha anthuwo...Yer 5:3wakantha nadzatimanga...Hos 6:1[onaninso: kanthidwa, likhidwa]

KANTHA (strike)mukanthe mtundu uwu uchite khungu...2 Maf 6:18ukanthe mbusa...Zek 13:7ndisafike ndi kukantha dziko lionongeke...Malak 4:6ndidzakantha mbusa ndipo zidzabalalika...Mat 26:31[onaninso: menya, panda, tentha, wamba]

KANTHA (struck)la Mulungu landikantha...Yob 19:21m’kukwiya kwanga ndinakantha...Yes 60:10munakantha mutu wa nyumba...Hab 3:13ndinakukanthani ndi chinsikwi...Hag 2:17[onaninso: menya, panda]

KANTHAWI (moment)chopepuka cha kanthawi...2 Akor 4:17[onaninso: mphindi]

Page 58: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KANTHIDWA (stricken) mtima wanga wakanthidwa...Mas 102:4[onaninso: kantha, likhidwa]

KAPADOKIYA (Cappadocia)Ayuda achokera kumeneku analipo pa tsiku la Pentekoste...Mac2:1,9akhristu akumeneku analankhulidwa ndi Petro...1 Pet 1:1

KAPERNAO (Capernaum)kwawo kwa Petro...Marko 1:21,29Yesu anachiritsa anthu kumeneko...Mat 8:5-17; 9:1-8;Marko1:21-28;Yoh 4:46-54Yesu analalikirako...Marko 9:33-50;Yoh 6:24-71kumagwiritsidwa ntchito ngati ku likulu...Mat 4:13-17ananeneredwa chiweruzo...Mat 11:23,24

KAPITAWO (aide)kapitawo wa kunyumba...Mac 12:20

KAPOLO (servant)adzakhala kapolo...Gen 9:25kapolo amalakalaka...Yob 7:2chidzasanduka kapolo...Miy 11:29kapolo wochita zinthu...Miy 17:2Israeli si kapolo...Yer 2:14kapolo amaopa mbuye...Mal 1:6[onaninso: mtumiki]

KAPOLO (slave)kuti munali akapolo...Deut 15:15wochita tchimo ndi kapolo...Yoh 8:34unali kapolo pamene Mulungu...1 Akor 7:21sindiwenso kapolo ai...Agal 4:7

KARIMELE (Carmel)mzinda wa Yuda...Yos 15:55malo a chipambano cha Saulo...1 Sam 15:12— phiri la ku Palestina...Yos 19:26malo amene Eliya anakhala nacho chipambano...1 Maf18:19-45unachezeredwa ndi Elisa...2 Maf 2:25

KASUPE (fountain)mwa iye kasupe wa madzi...Yoh 4:14

KASUPE (spring)amafanafana ndi kasupe...Miy 25:26ngati kasupe wochingidwa...Nyi 4:12kasupe wake adzaphwa...Hos 13:15kasupe amatulukitsa madzi...Yak 3:11[onaninso: meretsera, oneka, phukira]

KATSWIRI (expert)ndiponso akatswiri a njirisi...Yes 3:3[onaninso: m’misiri, waluso]

KATUNDU (burden)kuti muike pa ine katundu...Num 11:11ndikhale kwa ine ndekha katundu...Yob 7:20katundu wake adzachoka pa phewa...Yes 10:27amene katundu wake anawakhalira...Zef 3:18ndi katundu wanga ali wopepuka...Mat 11:30sindikusanjikani katundu...Chiv 2:24[onaninso: chinthenda, kukoka, lemetsa, nkhawa]

KATUNDU (goods)pochuruka katundu, akudyapo churukanso...Mlal 5:11ndi kufunkha akatundu ake...Mat 12:29[onaninso:chuma, zanga, zinthu]

KATUNGURUME (almond)

zopangika ngati katungurume...Eks 25:33[onaninso: mchiu]

KAVALO (horse)akavalo pamodzi ndi okwerapo...Eks 15:1amene umapatsa mphamvu kavalo...Yob 39:19pa kavalo wankhondo...Mas 33:17mphamvu za kavalo saziyesa...Mas 147:10kavalo amamkozera tsiku...Miy 21:31nditayang’ana ndinaona kavalo...Chiv 6:2ndinaona kavalo wakuda...Chiv 6:5ndinaona kavalo wotuwa...Chiv 6:8kavalo woyera mkuoneka...Chiv 19:11

KAVALO (horses)mkamwa mwa kavalo...Yak 3:3

KAYAFA (Caiphas)mpongozi wa Anasi; wamkulu wansembe...Yoh 18:13ananena uneneri... Yoh 11:49-52Yesu anaonekera kwa iye kuti aweruzidwe... Yoh 18:23,24atumwi anaonekera pamaso pake...Mac 4:1-22

KAYIKA (doubt)chikhulupiriro chochepawe, unakayikiranji...Mat 14:31[onaninso: wanjiranjira]

KAYIKA (doubting)mokhulupirira ndi mosakayika...Yak 1:6

KEBARA (Chebar)mtsinje wa ku Babulo...Ezek 1:3malo omwe Ezekiele ansaonera masomphenya ake...Ezek10:15,20

KEDORILAOMERE (Chedorlaomer)mfumu ya ku Elamu; anagonjetsa Kenani...Gen 14:1-16

KEFA (Cephas)dzina lachi Aramaiki la Petro... Yoh 1:42

KEKE (cake)Aefuremu ali ngati keke...Hos 7:8

KEMOSI (Chemosh)Mulungu wa a Moabu...Num 21:29ana amaperekedwa nsembe kwa iye...2 Maf 3:26,27Solomoni anamanga maguwa kwa iye...1 Maf 11:7Yosiya anawononga maguwa ake ...2 Maf 23:13

KERUBI (cherub)adakwera pa mkerubi...2 Sam 22:11

KHALA NDI PAKATI (conceive)ndipo taona, udzakhala ndi pakati...Luk 1:31[onaninso: ima]

KHALA (abide)safuna kukhala mkuwalako...Yob 24:13ndani angathe kukhala m’nyumba mwanu...Mas 15:1akhale pampamdo wake wa ufumu...Mas 61:7iye amene akhala pansi m’gaka yake...Mas 91:1ngati mukhala inu m’mau anga...Yoh 8:31koma kapolo sakhala mnyumba nthawi yonse...Yoh 8:35kuti akhale ndi inu kunthawi yonse...Yoh 14:16khalani mwa ine, ndi ine mwa inu...Yoh 15:4ngati mukhala mwa ine...Yoh 15:7khalani mchikondi changa...Yoh 15:9nanga chikondi cha Mulungu chikhala mwa iye bwanji?...1 Yoh3:17m’menemo tidziwa kuti tikhala mwa iye...1 Yoh 4:13[onaninso: tsala]

Page 59: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KHALA (abides)ndiye wokhalabe chiyambire kale...Mas 55:19wakukhala mwa ine...Yoh 15:5mau a Mulungu amoyo ndi okhalitsa...1 Pet 1:23amene achita chifuniro cha Mulungu akhala ku...1 Yoh 2:17

KHALA (abiding)ndipo mulibe mau okhala mwa inu...Yoh 5:38alibe moyo wosatha wakukhala mwa iye...1 Yoh 3:15

KHALA (became)munthuyo anakhala wamoyo...Gen 2:7ndipo kwa Ayuda ndinakhala...1 Akor 9:20khalani monga ine...Agal 4:12

KHALA (being)munthuyo nakhala...Gen 2:7zomlemekeza pokhala ndiripo...Mas 104:33pakuti mwa iye tikhala...Mac 17:28pokhala nao maonekedwe...Afil 2:6

KHALA (coal)ali ndi khala la moto...Yes 6:6sudzakhala khala loothako...Yes 47:14

KHALA (continue)anali chikhalire m’chiphunzitso...Mac 2:42akadakhala a ife akadakhalabe...1 Yoh 2:19zonse zikhala monga chiyambire...2 Pet 3:4akhala iye nthawi yosatha...Aheb 7:24[onaninso: khalabe, khama]

KHALA (dwell)Yehova, mwandikhazikitsa ine...Mas 4:8ndani angathe kukhala nyumba...Mas 15:1munthu ameneyo adzakhaladi...Mas 25:13khala m’dziko ndi kutsata...Mas 37:3kuti mudzakhale kumeneko...Mas 68:18kupambana kukhala masiku...Mas 84:10kuti ulemerero wake ukhale...Mas 85:9chifukwa ndimakhala pakati...Mas 120:5adzakhala pa malo otetezedwa...Yes 33:16ku Ejipito kukakhala nao...Yes 52:4ndimakhala pa malo aulemu...Yes 57:15asadzakhalenso ndi ife...Mali 4:15imalowa nkukhazikika momwemo...Mat 12:45ndi inu nonse okhala ku Yerusalemu...Mac 2:14ndidzakhazikika mwa iwo...2 Akor 6:16Khristu akhazikike m’mitima...Aef 3:17wonse ukhalemo mwa Khristuyo...Akol 1:19mau a Khristu akhazikike...Akol 3:16malo okhalamo Mulungu...Chiv 21:3adathawa namakhala...Mac 7:29

KHALA (dwelling)anthu okhala pa okha...Num 23:9njira yopita kumene kumakhala...Yob 38:19kuti mukhale nyumba...Aef 2:22ankakhala m’mahema...Aheb 11:9

KHALA (dwells)iye amene amakhala m’linga...Mas 91:1koma atate amene amakhala mwa...Yoh 14:10koma uchimo umene umakhala mwa ine...Aro 7:17Mzimu wa Mulungu akhaladi...Aro 8:9akamakhala mwa inu...Aro 8:11umulungu wonse umakhala...Akol 2:9m’mene chilungamo chizidzakhalamo...2 Pet 3:13kumene amakhala satana...Chiv 2:13

KHALA (dwelt)

Yakobe anakhala mlendo...Mas 105:23nadzakhala pakati pathu...Yoh 1:14ankakhala ngati mlendo...Aheb 11:9

KHALA (exist)mwachifuniro chanu zinakhala...Chiv 4:11[onaninso: ziripo]

KHALA (lying)anaona nsalu zabafuta zitakhala, komatu sanalowamo...Yoh

20:5[onaninso: bodza, nama, gona]

KHALA (obtain)kukondwa kosatha kudzakhala pa...Yes 35:10[onaninso: landira, peza]

KHALA (possess)mudzakhala nawo moyo...Luk 21:19wa inu adziwe kukhala nacho...1 Ates 4:4[onaninso: gonjetsa, landira]

KHALA (sit)anthu okhala pa...Mas 69:12tsiku la kukhala pa fumbi...Yes 47:1chifukwa chiyani tikungokhala...Yer 8:14munthu kuti akhale...Mat 20:23alembi ndi Afarisi akhala pa mpando wa Mose...Mat 23:2khala kudzanja langa...Aheb 1:13khalani apa pabwinopa...Yak 2:3kukhala nane pamodzi...Chiv 3:21ndikhala ine mfumu osati...Chiv 18:7

KHALA (sits)Mulungu amakhala pa...Mas 47:8amene amakhala pa mpando...Yes 40:22kotero kuti iye wakhala pansi ...2 Ates 2:4wadama uja wakhalapo...Chiv 17:15

KHALA (sitting)pamene ndikukhala pansi...Mas 139:2atakhala kudzanja lamanja...Marko 14:62kumene Khristu akukhala...Akol 3:1

KHALA (stand)nudzakhala chikhalire...Dan 2:44[onaninso: chirimika, ima, khazikika, limba, tsimikizidwa, uka]

KHALA CHIKHALIRE (endure)koma Yehova akhala chikhalire...Mas 9:7[onaninso: khala kosatha, pirira]

KHALA CHIKHLIRE (endures)koma mau a Mulungu akhala chikhalire...1 Pet 1:25[onaninso: pirira]

KHALA KOSATHA (endure)dzina lake lidzakhala kosatha...Mas 72:17[onaninso: khala chikhalire, pirira]

KHALA NDI MOYO (alive)ali ndi moyo...Num 16:33Mulungu wanu muli ndi moyo...Deut 4:4ndikhalitsanso ndi moyo...Deut 32:39kumanda ali a moyo...Mas 55:15adzapulumutsa moyo...Ezek 18:27kuti ali moyo...Marko 16:11wakhalanso moyo...Luk 15:24adzadziwonetsa wa moyo...Mac 1:3okhala ndi moyo...Aro 6:11kale ndinali ndi moyo...Aro 7:9akhalitsa ndi moyo...1 Akor 15:22

Page 60: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

adapatsa moyo...Aef 2:5anakupatsani moyo...Akol 2:13okhala ndi moyo...1 Ates 4:15wopatsidwa moyo...1 Pet 3:18ndi wamoyo...Chiv 1:18lakuti uli ndi moyo...Chiv 3:1anaponyedwa ali ndi moyo...Chiv 19:20

KHALA NDI MOYO (live)ndi kudya, ndi kukhala ndi moyo...Gen 3:22adzakhala nao ndi moyo...Lev 18:5sindidzakhala ndi moyo...Yob 7:16khalani okondwa ndi mkazi umkonda...Mlal 9:9anthu akhala ndi moyo...Yes 38:16adzakhala ndi moyo ndithu...Ezek 3:21ndipo mudzakhala ndi moyo...Amo 5:4wolungama adzakhala ndi moyo...Habak 2:4munthu sadzakhala ndi moyo...Mat 4:4iyeyu adzakhala ndi moyo...Yoh 6:57mwa iye tikhala ndi moyo...Mac 17:28khalani ndi mtendere ndi anthu onse...Aro 12:18koma ndiri ndi moyo wosatinso ine ai...Agal 2:20ngati tili ndi moyo ndi Mzimu...Agal 5:25kukhala ndi moyo ndiko Khristu...Afil 1:21kukhala opembedza m’moyo...2 Tim 3:12koma akakhale ndi moyo...1 Pet 4:6

KHALA NDI MOYO (lives)munthu sakhala wa moyo...Deut 8:3wamoyo, akhala wamoyo...Aro 6:10wa ife adzakhalira ndi moyo...Aro 14:7[onaninso: moyo]

KHALA MASO (awake)koma mtima wanga unali maso...Nyi 5:2khala maso ogona iwe...Aef 5:14[onaninso: dikira, galamuka, kumika, uka]

KHALA FUMBI (destruction)mubweza munthu akhale fumbi...Mas 90:3[onaninso: chiwonongeko, ononga, onongeka, pasula]

KHALA WOSALAKWA (blameless)mukhale opanda chifukwa...1 Akor 1:8wokhala wosalakwa ine...Afil 3:6yopanda chifukwa...1 Ates 3:13[onaninso: ngwiro, opanda chilema, panda chilema]

KHALABE (continue)tidzakhalabe muuchimo kodi...Aro 6:1wosakhala m’zonse zolembedwa...Agal 3:10iwo sanakhalabe m’pangano langa...Aheb 8:9chikondi cha pa abale chikhalebe...Aheb 13:1[onaninso: khala, khama]

KHALIDWE (behavior)azikhala ndi makhalidwe oyenera...Tit 2:3[onaninso: longosoka]

KHAMA (continue)chitani khama m’kupemphera...Akol 4:2[onaninso: khala, khalabe]

KHAMA (diligence)munthu wakhama amapeza...Miy 12:27khama lalikuru lanji...2 Akor 7:11kuyesa mwa khama la ena...2 Akor 8:8

KHAMA (diligent)dzanja la a khama...Miy 10:4ogwira ntchito mwakhama...Miy 12:24munthu wakhama amalemera...Miy 13:4

[onaninso: changu]

KHAMU (company)ndiwo khamu lalikulu...Mas 68:11[onaninso: mayanjano, unyinji]

KHANDA (baby)pakuti ali khanda...Aheb 5:13[onaninso: mwana]

KHAZIKIKA (convinced)munthu aliyense akhazikike...Aro 14:5

KHAZIKIKA (established)dziko lapansi lakhazikika...1 Mbir 16:30likhazikike lonjezano lanu la kwa Davide...2 Mbir 1:9nakhazika mayendedwe anga...Mas 40:2anakhazika mboni kwa Yakobo...Mas 78:5ukhazikika nthawi zonse...Miy 12:19la nyumba ya Yehova lidzakhazikika...Yes 2:2ndi okhazikika mchikhulupiriro...Akol 2:7limene likhazikika pamalonjezano...Aheb 8:6mtima ukhazikike ndi chisomo...Aheb 13:9wakutikhazika pamodzi ndi inu...2 Akor 1:21[onaninso: khazikitsa]

KHAZIKIKA (stand)pa uwu wokha sukhoza kukhazikika...Marko 3:24[onaninso: chirimika, ima, khala, limba, tsimikizidwa, uka]

KHAZIKITSA (establish)ndipo ndidzakhazikitsa...Ezek 16:60mukhazikitse chilungamo...Amo 5:15pofuna kukhazikitsa chilungamo...Aro 10:3amene adzakukhazikitsani...2 Ates 3:3inunso khazikani mtima...Yak 5:8nadzakukhazikitsani pa maziko...1 Pet 5:10kuwakhazika kosatha...2 Mbir 9:8ndidzakhazikitsa zidzukulu zako...Mas 89:4mutikhazikitsire ife ntchito...Mas 90:17[onaninso: limbitsira]

KHAZIKITSA (established)mudaukhazikitsa kuyambira makedzana...Mas 93:2mfumu akhazikitsa dziko...Miy 29:4nakhazikitsa dziko lapansi...Yer 10:12[onaninso: khazikika]

KHETSA MWAZI (bloodthirsty)munthu wokhetsa mwazi...Mas 5:6anthu okhetsa mwazi...Mas 55:23

KHOKA (net)ndiponya makoka...Luk 5:5ponyani khoka kumbali...Yoh 21:6[onaninso: ukonde]

KHOLA (fold)zimene sizili za m’khola lino...Yoh 10:16[onaninso: pinda]

KHOMO (door)uchimo ubwatama pakhomo...Gen 4:7sungani pakhomo pa milomo yanga...Mas 141:3nakunkhunizira mwala waukuru pakhomo la manda...Mat 27:60ine ndine khomo la nkhosa... Yoh 10:7pakuti panditsegukira pakhomo lalikulu ndi lochititsa...1 Akor16:9padanditsegukira kwa ine pakhomo, mwa Ambuye...2 Akor

2:12taonani, woweruza waima pakhomo...Yak 5:9ndapatsa pamaso pako khomo lotseguka...Chiv 3:8

Page 61: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

taona ndaima pakhomo ndigogoda...Chiv 3:20ndipo taonani khomo lotseguka m’mwamba...Chiv 4:1[onaninso: chitseko]

KHOMO (gate)khomo lakachisi lotchedwa Lokongola...Mac 3:2[onaninso: chipata, chitseko]

KHOMO LOLOWERA (entrance)adzakutsekulirani kwathunthu khomo lolowera...2 Pet 1:11[onaninso: potsegulira]

KHOSI (neck)ndiponso pakhosi pake posalala...Gen. 27:16moyo ndi khosi lako...Miy 3:22khosi lako liri mtsempha...Yes 48:4ikolowekedwe m’khosi mwake...Mat 18:6namkupatira pakhosi pake...Luk 15:20

KHOSI (necks)naumitsa khosi lao...Neh 9:29anapereka khosi lao...Aro 16:4[onaninso: makosi]

KHOZA (could)wachita chimene wakhoza...Marko 14:8ndingakhale ndikhoza...1 Akor 13:2anakhoza kuliwerenga...Chiv 7:9

KHRISTU (Christ)Yesu Khristu makolo ake anali...Mat. 1:1Yesu wotchedwa Khristu...Mat 1:16inu ndinu Khristu, mwana wa Mulungu...Mat 16:16kuti utiuze ife ngati ndiwe Khristu...Mat 26:63amene ndi Khristu Ambuye...Luk 2:11iye yekha ndiye Khristu mfumu...Luk 23:2Khristu akhala ku nthawi yonse...Yoh 12:34ali ndi mzimu wa Khristu...Aro 8:9Khristu Yesu ndi amene anafa...Aro 8:34pakuti Khristunso sanadzikondweretse...Aro 15:3kodi Khristu wagawika...1 Akor 1:13koma kwa Iye muli inu mwa Khristu...1 Akor 1:30adakulunzanitsani ndi Khristu...Agal 2:17ndidapachikidwa pa mtanda pamodzi ndi Khristu...Agal 2:20ndi Khristu amene ali ndi moyo mwa ine...Agal 2:20mbeu yako ndiye Khristu...Agal 3:16Khristu akhazikike m’mitima mwanu...Aef 3:17ndipo Khristu adzakuwalira...Aef 5:14monga momwe Khristu ali mutu wa mpingo...Aef 5:23moyo ndi Khristu amene...Afil 1:21Yesu Khristu ndi Ambuye...Afil 2:11ndingathe kuchita zonse chifukwa cha Khristu...Afil 4:13chinsinsicho nchakuti Khristu...Akol 1:27Khristu ndiye moyo wanu...Akol 3:4koma Khristu basi...Akol 3:11munthu uja timati Khristu...1Tim 2:5Yesu Khristu ndi yemweyo...Aheb 13:8wokhulupirira kuti Yesu ndiye Khristu...1Yoh 5:1ndi ulamuliro wa Khristu wake...Chiv 12:10nachita ufumu pamodzi ndi Khristu...Chiv 20:4

KHUDZA (cling)usandikhudze pakuti sindinatha...Yoh 20:17[onaninso: gwira, matirira]

KHULULUKA (despaired)ndinatembenuka ndi kukhululuka za ntchito...Mlal 2:20[onaninso: ida nkhawa]

KHULULUKIDWA (forgiven)zolakwa zake zakhululukidwa...Mas 32:1Mulungu angawakhululukire...Marko 4:12

munthu amene wakhululukidwa zochepa...Luk 7:47adatikhululukira machimo athu...2 Akor 2:10Ambuye adzamkhululukira machimo...Yak 5:15Mulungu wakukhululukirani machimo...1 Yoh 2:12

KHULULUKIRA (forgave)mudakhululukiradi mlandu wa...Mas 32:5adawakhululukira ngongolezo...Luk 7:42muzikhululukirana monga momwe...Aef 4:32monga Ambuye adakukhululukirani...Akol 3:13

KHULULUKIRA (forgives)amene akhululukira mphulupulu...Mas 103:3amene akhululukiranso machimo...Luk 7:49

KHULULUKIRA (forgive)mukhululuke ndipo muchitepo kanthu...1 Maf 8:39ndidzawakhululukira zoipa zao...2 Mbir 7:14mumakhululukira anthu anu...Mas 86:5mutikhululukire ife machimo athu...Mat 6:12ngati mukhululukira anthu machimo...Mat 6:14ngati simukhululukira anthu machimo...Mat 6:15akapanda kukhululukira mbale...Mat 18:35ndani angakhululukire machimo...Marko 2:7amene mudzawakhululukira machimo...Yoh 20:23nkwabwino mukhululukire...2 Akor 2:7mukakhululukira munthu, inenso...2 Akor 2:10ndikhululukireni kulakwa kwangaku...2 Akor 12:13adzatikhululukira machimo athu...1 Yoh 1:9

KHULULUKIRANA (forgiving)mtima wachifundo, akukhululukirana...Aef 4:32kukhululukirana eni okha...Akol 3:13

KHULUPIRIKA (faithful)ndiye Mulungu wokhulupirika...Deut 7:9pakuti okhulupirika achepa...Mas 12:1Yehova asunga okhulupirika...Mas 31:23ayang’ana okhulupirika m’dziko...Mas 101:6angapeze munthu wokhulupirika...Miy 20:6yoona ndi yokhulupirika...Yer 42:5ndiye Woyera wokhulupirika...Hos 11:12kodi ali kapolo wokhulupirika ndi wanzeru...Mat 24:45iye amene akhulupirika...Luk 16:10ngati simunakhala okhulupirika...Luk 16:12mwandiyesera ine wokhulupirika...Mac 16:15Mulungu ali wokhulupirika amene...1 Akor 1:9ndi wokhulupirika mwa Ambuye...1 Akor 4:17koma Mulungu ali wokhulupirika...2 Akor 1:18abale okhulupirika mwa Khristu...Akol 1:2wakuitana inu ali wokhulupirika...1 Ates 5:24mauwa ali okhulupirika...1 Tim 1:15wachifundo ndi wokhulupirika...Ahe 2:17amene anakhala wokhulupirika...Ahe 3:2wolonjezayo ali wokhulupirika...Aheb 10:23ali wokhulupirika ndi wolungama...1 Yoh 1:9khala wokhulupirika kufikira imfa...Chiv 2:10mau awa ali okhulupirika ndi oona...Chiv 21:5

KHULUPIRIRA (believe)khulupirirani aneneri ake...2 Mbir 20:20anafuula nanena, ndikhulupirira...Marko 9:24khulupirirani kuti mwazilandira...Marko 11:24akhulupirira kanthawi...Luk 8:13mtima kusakhulupirira zonse...Luk 24:25kwa iwotu akukhulupirira dzina...Yoh 1:12mudzakhulupirira bwanji...Yoh 3:12simukhulupirira ameneyo...Yoh 5:38kuti tione ndikukhulupirira...Yoh 6:30kodi ukhulupirira mwana wa Mulungu...Yoh 9:35

Page 62: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kuti akhulupirire kuti inu munandituma...Yoh 11:42khulupirirani inenso...Yoh 14:1kuti mukakhulupirire kuti Yesu ndi Khristu...Yoh 20:31mfumu Agripa, mukhulupirira...Mac 26:27ndi kukhulupirira mumtima mwako...Aro 10:9ndipo adzakhulupirira bwanji iye amene...Aro 10:14mkazi wosakhulupirira...1 Akor 7:12ifenso tikhulupirira...2 Akor 4:13likapatsidwe kwa okhulupirira...Agal 3:22sikukhulupirira kwa iye kokha...Afil 1:29ayenera kukhulupirira kuti...Aheb 11:6ukhulupirira iwe kuti Mulungu ali m’modzi...Yak 2:19ziwanda zikhulupiriranso, ndipo...Yak 2:19okondedwa musamakhulupirire mzimu uliwonse ...1 Yoh 4:1[onaninso: vomereza]

KHULUPIRIRA (believed)ndipo amakhulupirira Yehova...Gen 15:6ndikadapanda kukhulupirira...Mas 27:13anthu Asamariya ambiri anakhulupirira...Yoh 4:39chifukwa wandiona ine wandikhulupirira...Yoh 20:29iwo amene anamva mau anakhulupirira...Mac 4:4ndipo unyinyi wa iwo akukhulupirira...Mac 4:32munalandira Mzimu Woyera pamene munakhulupirira...Mac19:2ndipo Abrahamu anakhulupirira Mulungu...Aro 4:3ndimdziwa iye amene ndamkhulupirira...2 Tim 1:12wachibwana akhulupirira mau onse...Miy 14:15amene akhulupirira nabatizidwa...Marko 16:16kuti yense wakukhulupirira iye...Yoh 3:16iye amene akhulupirira mwanayo...Yoh 3:36pakuti ndi mtima munthu akhulupirira...Aro 10:10chikhulupirira zinthu zonse...1 Akor 13:7

KHULUPIRIRA (believing)ndikhulupirira mudzalandira...Mat 21:22ndi Abrahamu wokhulupirirayo...Agal 3:9

KHULUPIRIRA (confidence)kupambana kukhulupirira munthu...Mas 118:8m’kukhulupirira mudzakhala mphamvu...Yes 30:15osakhulupirira thupi...Afil 3:3[onaninso: kulimba mtima]

KHUMBA (desire)udzakhumba mwamuna wako...Gen 3:16chokhumba oipa chidzatayika...Mas 112:10moyo wathu ukhumba dzina lanu...Yes 26:8[onaninso: chikhumbo, chilakolako, funitsitsa, lakalaka]

KHUMBA (desires)kuzikhumbira kupambana golide...Mas 19:10mwa inu amakhumba moyo...Mas 34:12zimene mtima wako ukhumba...Mas 37:4ndimakhumbitsa ndi mtima wanga...Aro 10:1[onaninso: funa, zilakolako]

KHUMI NDI M’MODZI (eleven)ana ake khumi ndi m’modzi...Gen 32:22ophunzira khumi ndi m’modzi aja...Mat 28:16ija la atumwi khumi ndi m’modzi...Mac 1:26

KHUMUDWA (offense)mwala wakukhumudwa nao...1 Pet 2:8[onaninso: chikhumudwitso,chokhumudwitsa, khumudwitsa,

lakwa,lakwitsa]

KHUMUDWITSA (offend)kuti ife tisawakhumudwitse...Mat 17:27anati kwa iwo kodi mukhumudwa...Yoh 6:61[onaninso: lakwa, palamula]

KHUMUDWITSA (offense)khalani osakhumudwitsa...1 Akor 10:32[onaninso: chikhumudwitso,chokhumudwitsa, khumudwa,

lakwa,lakwitsa]

KHUNGU (blind)ndipo pamene mupereka ya khungu...Mal 1:8unachititsa khungu maganizo ao...2 Akor 4:4[onaninso: akhungu, wakhungu]

KHUTA (filled)ludzu la chilungamo chifukwa adzakhuta...Mat 5:6baleka athange akhuta ana...Marko 7:27ndipo analakalaka kukhutitsa mimba...Luk 15:16mukafunde ndi kukhuta...Yak 2:16[onaninso: dzadzidwa, dzadza, dzala]

KHUTA (fullness)adzakhuta kwambiri ndi zonona...Mas 36:8[onaninso: chidzalo, kudzala, kudzaza, kwaniridwa,

makwaniridwe]

KHUNGUBWI (raven)kwa ana a khungubwi...Mas 147:9[onaninso: khwangwala]

KHUTIRA (content)ndaphunzira kukhutira...Afil 4:11zimene muli nazo mukhutira nazo...Aheb 13:5[onaninso: kwanira]

KHUTIRA (contentment)munthu akakhutira ndi zimene ali...1 Tim 6:6

KHUTITSIDWA (abased)chinsinsi chake cha kukhala wokhutitsidwa...Afil 4:12

KHUTU (ear)ndipo amuboole khutu lake...Eks 21:6kodi suja khutu ndiye limamva...Yob 12:11tcherani khutu kuti mundimve...Mas 31:2khutu la anzeru lifunitsa...Miy 18:15nagalamutsa khutu langa...Yes 50:4khutu lao liri losadulidwa...Yer 6:10chimene muchimva m’khutu...Mat 10:27mpaka kumusenga khutu...Yoh 18:10ndi khutu silinazimva...1 Akor 2:9ndipo ngati khutu likati...1 Akor 12:16wokhala nalo khutu amve...Chiv 2:7

KHUTU (ears)chidzamuliritsa mwini khutu...2 Maf 21:12komatu poyabwa m’khutu...2 Tim 4:3[onaninso: makutu]

KHWANGWALA (raven)khwangwala amampatsa chakudya...Yob 38:41ngati nthenga za khwangwala...Nyi 5:11onani makwangwala, safetsa...Luk 12:24[onaninso: khungubwi]

KHWIMA (mature)pakati pa anthu okhwima...1 Akor 2:6maganizo anu, mukhale okhwima...1Akor 14:20amene tili okhwima pa moyo...Afil 3:15

KILIYONI (Chilion)mwana wamwamuna wa Elimeleki...Rut 1:2anali mwamuna wa Olipa...Rut 1:4,5Bowazi adagula katundu wake...Rut 4:9

Page 63: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KINERETI (Chinnereth)mzinda wozungulira Nafutali...Deut 3:17dera lozungulira nyanja ya Galileya...1 Maf. 15:20chimodzimodzinso ndi malo athyathyathya a Genesarete...Mat14:34— dzina la mchipangano chakale la nyanja ya Galileya...Num34:11yotchedwa nyanja ya Genesarete...Luk 5:1

KINIYU (Coniah)mfumu ya Yuda...Yer 22:24,28chimodzimodzinso ndi Yehoyakini...2 Maf 24:8

KOBIRI (coin)sizigulidwa ka kobiri...Mat 10:29[onaninso: ndalama]

KODWA (ensnared)munthu woipa amakodwa...Miy 12:13msilikali sakodwa nazo...2 Tim 2:4[onaninso: agwa]

KODWA (snared)oipa akodwa mu msampha...Mas 9:16adzakodwa mu msampha...Yes 8:15

KOKERA (enticed)chilakolako cha iye mwini chimkokera...Yak 1:14ndi kukoka kwa mau ake...Miy 7:21

KOKOMA (roar)nyanja ikokome pamodzi...1 Mbir 16:32ngakhale nyanja zikokome...Mas 46:3[onaninso: bangula]

KOLA (catch)kuti akamkole Iye m’kulankhula kwake...Marko 12:13[onaninso: gwira, sodza]

KOLA (entangle)nakhala upo wakumkola iye...Mat 22:15

KOLOLA (reap)akulira, adzakolola akufuula...Mas 126:5ndipo amakolola kamvulumvulu...Hos 8:7sizifetsa kapena kukolola...Mat 6:26ndimakolola kumene sindidabzyale...Mat 25:26amabzyala, adzakolola zomwezo...Agal 6:7pa nthawi yake tidzakolola...Agal 6:9koma adakolola minga...Yer 12:13ndipo mudakolola chilango...Hos 10:13

KOLOSE (Colosse)mzinda ku Asiya wamng’ono...Akol 1:2analalikidwa ndi Epafra...Akol 1:7sunachezeredwe ndi Paulo...Akol 2:1Paulo analemba za mavuto ndi zolakwitsa za mzindaumenewu...Akol 2:16-23

KOLOWOLA (plucked)mukadakolowola maso anu ndi kundipatsa...Agal 4:15[onaninso: kudzula, thyola]

KOMA (beauty)zaulemelero ndi zokoma...Eks 28:2[onaninso: chisomo, kongoletsa, kukongola, ulemelero]

KOMA (pleasant)zingakhale zokoma kudya...Gen 3:6adanyoza dziko lokoma...Mas 106:24ati kukoma...Mas 133:1

[onaninso: bwino, chofunika, kometsera, kondwera,kondweretsa]

KOMA (well)podzichitira wekha zokoma...Mas 49:18[onaninso: bwino,chitsime, komera, limba, ngwiro, pulumutsa]

KOMERA (acceptable)nthawi imene ndinakukomera mtima ndinakukha...Yes 49:8ndikalalike chaka chokomera Yehova...Yes 61:2[onaninso: kondweretsa, landiridwa, landirika, sankhika]

KOMERA (favourable)sadzandikomera mtima...Mas 77:7mudakomera mtima...Mas 85:1

KOMERA (favoured)Mulungu wakukomerani mtima...Luk 1:28[onaninso: kondwera]

KOMERA (pleasure)monga umo kunakomera chifuniro chake...Aef 1:5nakakwaniritse chomkomera chonse...2 Ates 1:11[onaninso: konda, kondwera, zikhumbitso]

KOMERA (well)kuti chikukomereni inu ndi ana anu akukutsatani...Deut 4:40nenani za wolungama kuti kudzamkomera iye...Yes 3:10[onaninso: bwino,chitsime, koma, limba, ngwiro, pulumutsa]

KOMERA MTIMA (favor)ndikukomerana mtima...Yob 10:12Yehova akomera mtima munthu...Miy 12:2nipempha kuti aikomere mtima...Yer 26:19anthu onse ankawakomera mtima...Mac 2:47[onaninso: chisomo, kukoma mtima]

KOMETSA (beautify)adzakometsa ofatsa ndi...Mas 149:4[onaninso: kongoletsa]

KOMETSA (glorify)ndidzakometsa nyumba ya...Yes 60:7[onaninso: chitira ulemu, lemekeza]

KOMETSEDWA (adorn)udzakometsedwa...Yer 31:4wokometsedwera mwamuna...Chiv 21:2[onaninso: kometsera, kongoletsa, nyezimiritsa]

KOMETSERA (adorn)anadzikometsera okha...1 Pet 3:5[onaninso: kometsedwa, kongoletsa, nyezimiritsa]

KOMETSERA (pleasant)mau okometsera ali ngati...Miy 16:24[onaninso: bwino, chofunika, koma, kondwera, kondweretsa]

KOMOKA (fainted)moyo wao unakomoka...Mas 107:5inde ukomokanso ndi...Mas 84:2moyo wanga unakomoka...Mas 119:81

KONDA (affection)pakuti ndimakukondani...Afil 1:8[onaninso: chikondi]

KONDA (favor)pofuna kukonda Ayuda...Mac 24:27[onaninso: chisomo, komera mtima, kukoma mtima]

KONDA (love)uzikonda mnansi wako...Lev 19:18

Page 64: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

muzikonda Yehova Mulungu...Deut 6:5mudzakonda zachabe ndi...Mas 4:2kondani Yehova, inu nonse...Mas 31:23mukonda chilungamo ndipo mudana...Mas 45:7andikondadi ndidzampulumutsa...Mas 91:14ndikondadi chilamulo chanu...Mas 119:97akukonda chilamulo chanu...Mas 145:20ngakhale kukonda ngakhale...Mlal 9:1ndidzawakonda mwa ufulu...Hos 14:4ndani wa iwo adzaposa kumkonda...Luk 7:42ngati mukonda ine, sungani...Yoh 14:15ndipo Atate wanga adzamkonda...Yoh 14:23kodi undikonda ine koposa awa...Yoh 21:15ukonda ine kodi...Yoh 21:16amuna inu, kondani akazi...Aef 5:25amuna inu, kondani akazi...Akol 3:19akazi ang’ono akonde amuna...Tit 2:4mungakhale simunamuona mumkonda...1 Pet 1:8kondani abale, opani Mulungu...1 Pet 2:17amene anakonda mphotho...2 Pet 2:15musakonde dziko lapansi...1Yoh 2:15tikondane wina ndi mnzake...1Yoh 4:7wosakonda sazindikira Mulungu...1 Yoh 4:8tikonda ife chifukwa anayamba...1Yoh 4:19amene akonda Mulungu akondenso...1Yoh 4:21sanakonda moyo wawo kufikira...Chiv 12:11[onaninso: chikondano, chikondi, kondana, kukondana]

KONDA (loved)Yehova anakonda Israeli...1 Maf 10:9kutali wondikonda ndi bwenzi...Mas 88:18ndakukondani, ati Yehova...Mal 1:2mukuti, mwatikonda motani...Mal 1:2chifukwa anakonda kwambiri...Luk 7:47Mulungu anakonda dziko lapansi...Yoh 3:16ananena, taonani anamkondadi... Yoh 11:36amene Yesu anamkonda, anali...Yoh 13:23monga momwe Atate wandikonda...Yoh 15:9nimunawakonda iwo monga momwe...Yoh 17:23kunalembedwa, ndinakonda Yakobo...Aro 9:13mwana wa Mulungu, amene anakonda...Agal 2:20monganso Khristu anakonda...Aef 5:25mwakonda chilungamo, ndi kukonda...Aheb1:9sikuti ife tinakonda Mulungu...1 Yoh 4:10ngati Mulungu anatikonda ife...1 Yoh 4:11iye amene atikonda ife...Chiv 1:5

KONDA (lovely)pokhala inu mpotikonda ndithu...Mas 84:1

KONDA (loves)ndiye wakukonda chilungamo...Mas 33:5moyo ndani, wokonda masiku...Mas 34:12bwenzi limakonda nthawi zonse...Miy 17:17iye wakukonda atate ake...Mat 10:37wokonda moyo wake adzautaya...Yoh 12:25iyeyu ndiye wondikonda ine...Yoh 14:21Mulungu akonda wopereka...2 Akor 9:7koteronso amuna azikonda akazi...Aef 5:28ngati wina akonda dziko lapansi...1 Yoh 2:15amene akonda Mulungu akondenso...1 Yoh 4:21yense wakukonda iye amene...1 Yoh 5:1

KONDA (pleasure)amakondetsa zosangalatsa...Miy 21:17Atate anu akonda kukupatsani...Luk 12:32[onaninso: komera, kondwera, zikhumbitso]

KONDANA (love)kondanani nao adani anu...Mat 5:44kuti mukondane wina ndi mnzake...Yoh 15:13chifukwa tikondana ndi abale...1 Yoh 3:14

tikondane wina ndi mnzake...1 Yoh 4:7tikakondana wina ndi mnzake...1 Yoh 4:10[onaninso: chikondano, chikondi, konda, kukondana]

KONDWA (merry)mtima wokondwa utsekeretsa...Miy 15:13kudya, kumwa ndikumadzikondweretsa...Mlal 8:15kuti tisangalale ndi kukondwera...Luk 15:32

KONDWA (rejoice)minda ikondwe pamodzi...1 Mbir 16:32anthu okutumikirani akondwe...2 Mbir 6:41anakondwa masiku onse...Mas 89:16tiyeni tikondwe ndi...Mas 118:24iwowa amakondwa pochita...Miy 2:14uzikondwa ndi mkazi wa...Miy 5:18tizisangalala kwambiri ndi kukondwa...Nyi 1:4anthu osauka adzakondwa...Yes 29:19mtima wanga ukukondwadi...Yes 61:10atumiki anga adzakondwa...Yes 65:13zapansi pano adzakondwa...Yoh 16:20mtima wanu udzakondwa...Yoh 16:22muzikondwa nawo amene akondwa...Aro 12:15pamenepo ine ndikukondwa...Afil 1:18choncho ndili wokondwa...Afil 2:17muzikondwa mwa Ambuye...Afil 4:4khalani okondwa nthawi zonse...1 Ates 5:16[onaninso: kondwera]

KONDWA (rejoiced)mtima wangawo unkakondwa...Mlal 2:10analiwonadi nakondwa...Yoh 8:56ndakondwa kwambiri mwa...Afil 4:10[onaninso: kondwera]

KONDWERA (delight)kodi Yehova akondwera...1 Sam 15:22kodi adzadzikondweretsa...Yob 27:10udzikondweretsenso mwa Yehova...Mas 37:4tiye tikondwere ndi chikondano...Miy 7:18ndi kukondwera pamaso pake...Miy 8:30moyo wanu nukondwere...Yes 55:2kuchita kukondwera kwako...Yes 58:13ine ndikondwera ndi chilamulo...Aro 7:22[onaninso: chikondwerero, kwezeka, sekeretsa]

KONDWERA (delighted)Yehova anakondwera nawo...Deut 10:15

KONDWERA (delights)bwenziwe, m’zokondweretsa...Nyi 7:6Yehova akondwera mwa iwe...Yes 62:4akondwera nacho chifundo...Mika 7:18

KONDWERA (enjoy)lidzakondwera nao masabata...Levitiko 26:34tsopano ndiyesepo zokondweretsa...Mlal 2:1koposa kukondwerera zosangalatsa...Aheb 11:25kuti tikondwere nazo...1 Tim 6:17[onaninso: sangalala]

KONDWERA (enjoyment)munthu azikondwerera moyo...Mlal 8:15

KONDWERA (favoured)popeza munakondwera nao...Mas 44:3[onaninso: komera]

KONDWERA (glad)ndidzakondwera ndi kusekera mwa inu...Mas 9:2nchifukwa chake mtima wanga ukukondwa...Mas 16:9sangalalani ndikukondwa inu nonse...Mas 32:11

Page 65: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ngalande zake zidzakondweretsa...Mas 46:4ndi vinyo wokondweretsa mtima wa...Mas 104:15ndinakondwera m’mene ananena nane...Mas 122:1kuti tisangalale ndikukondwerera...Luk 15:32Abrahamu anakondwera kuona tsiku langa...Yoh 8:56

KONDWERA (pleasant)moyo wako udzakondwera...Miy 2:10[onaninso: bwino, chofunika, koma, kometsera, kondweretsa]

KONDWERA (pleased)mwana amene ndimakondwera...Miy 16:7pamenepo mudakondwera ndi...Mas 51:19ndimakondwera naye...Mat 3:17[onaninso: kondweretsa]

KONDWERA (pleasure)Mulungu wokondwerera...Mas 5:4monga mwa kukondwera kwanu...Mas 51:18pakuti atumiki anu akondwera...Mas 102:14Mulungu sakondwera nazo...Mlal 5:4mupeza kukondwerera kwanu...Yes 58:3kuchita kukondwerera kwako...Yes 58:13woipa ine ndimakondwera naye...Ezek 18:23sindikukondwera nanu...Mal 1:10iye wakutsata zomkondweretsa...1 Tim 5:6sidakondwere nazo...Aheb 10:6ine sindikondwera naye...Aheb 10:38ndipo mwachita zokukondweretsani...Yak 5:5[onaninso: komera, konda, zikhumbitso]

KONDWERA (pleasures)zokondweretsa za moyo uno...Luk 8:14kukondwerera zosangalatsa...Aheb 11:25[onaninso: zokondweretsa]

KONDWERA (rejoice)othawira kwa inu akondwere...Mas 5:11Yakobe adzakondwera...Mas 14:7kondwerani mwa Chauta...Mas 33:1amene amakondwera poona...Mas 35:26munthu wangwiro adzakondwera...Mas 58:10koma mfumu idzakondwera...Mas 63:11anthu anu Mulungu, akondwere...Mas 68:3zapansi pano zikondwere...Mas 96:11pa dziko lapansi akondwere...Mas 97:1muzikondwerera unyamata wanu...Mlal 11:9ndidzakondwera kuwachitira zabwino...Yer 32:41adzakondwera nawe poimba...Zef 3:17muzikondwera kuti maina anu...Luk 10:20bwenzi mutakondwera kuti...Yoh 14:28mumakondwera ndi chimwemwe...1 Pet 1:8[onaninso: kondwa]

KONDWERA (rejoiced)adzakondwera nanu kuti mwakhoza...Deut 30:9ukukondwera mwa Mulungu...Luk 1:47kotero kudakondweretsa...Luk 10:21[onaninso: kondwa]

KONDWERA (rejoices)mtima wanga ukukondwa...Mas 16:9koma chimakondwerera choona...1 Akor 13:6

KONDWERA (rejoicing)ndi kufuula mokondwera...Mas 107:22nyimbo zokondwerera...Mas 118:15ndizo zokondweretsa mtima...Mas 119:111ndi kufuula mokondwera...Mas 126:6ndi kumakondwa nawo ana...Miy 8:31anapita njira yake wokondwera...Mac 8:39komabe ndife okondwa...2 Akor 6:10

[onaninso: chimwemwe, kudzitamandira]

KONDWERETSA (acceptable)zabwino, zangwiro ndizomkondweretsa...Aro 12:2kuyesera chokondweretsa...Aef 5:10nacho Mulungu mom’kondweretsa...Aheb 12:28[onaninso: komera, landiridwa, landirika, sankhika]

KONDWERETSA (pleasant)ndiye mwana wokondweretsa...Yer 31:20[onaninso: bwino, chofunika, koma, kometsera, kondwera]

KONDWERETSA (please)makhalidwe a munthu akondweretsa...Miy 16:7ndimachita zonkondweretsa...Yoh 8:29sangathe kukondweretsa...Aro 8:8mwa ife azikondweretsa...Aro 15:2m’mene angankondweretsere...1 Akor 7:32ndikadayesabe kukondweretsa...Agal 1:10nkosatheka kukondweretsa Mulungu...Aheb 11:6

KONDWERETSA (pleased)Mulungu sadakondwere nawo...1 Akor 10:5anali wokondweretsa Mulungu...Aheb 11:5amene ndimakondwera naye...2 Pet 1:17[onaninso: kondwera]

KONDWERETSA (pleasing)nsembe yolandirika, yokondweretsa...Afil 4:18kutero kumakondweretsa...Akol 3:20chomkondweretsa pamaso pake...Aheb 13:21

KONGOLA (beautiful)anali wokoma thupi ndi wokongola...Gen 29:17mzinda wokongola wa Ziyoni...Mas 48:2chinthu chiri chonse anachikongoletsa...Mlal 3:11wakongola, bwenzi langa...Nyi 6:4ya Yehova idzakhala yokongola...Yes 4:2ha, akongolatu pa mapiri...Yes 52:7amene amaoneka okongola...Mat 23:27amakhala pa khomo lokongola...Mac 3:10anaona kuti anali okongola...Aheb 11:23

KONGOLA (borrows)woipa akongola...Mas 37:21

KONGOLA (comeliness)alibe maonekedwe, pena kukongola...Yes 53:2

KONGOLA (owe)unakongola chiyani kwa ine...Luk 16:5[onaninso: ngongole]

KONGOLA (owed)amene anali ndi ngongole...Mat 18:24adaamkongoza ndalama...Mat 18:28amene adaakongola ndalama...Luk 7:41

KONGOLETSA (adorn)inde adzikongoletse...1 Tim 2:9[onaninso: kometsedwa, kometsera, nyezimiritsa]

KONGOLETSA (beautify)adzabwera nayo kuti akongoletsere...Yes 60:13[onaninso: kometsa]

KONGOLETSA (beauty)kudzikongoletsa kwanu...1 Pet 3:3koma kudzikongoletsa kwanu...1 Pet 3:4[onaninso: chisomo, koma, kukongola, ulemelero]

KONGOLETSA (lend)

Page 66: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ukongoletsa ndalama anthu...Eks 22:25kumkongoletsa ndithu zofikira...Deut 15:8ngati mukongoletsa kanthu kwa...Luk 6:34[onaninso: bwereka]

KONKHA (washed)anakonkha mapazi anga...Luk 7:44[onaninso: chapa, masula, sambitsa, sambitsidwa, tsuka]

KONZA (adorn)mukonza manda...Mat 23:29anakonzedwa ndi...Luk 21:5

KONZA (amend)konzani makhalidwe ndi zochita...Yer 7:3konzani makhalidwe anu...Yer 35:15

KONZA (clean)kusamba m’mwemo, ndikukonzeka...2 Maf 5:12ngati mufuna mungathe kundikonza...Mat 8:2mwakhala okonzeka tsopano...Yoh 15:3[onaninso: yera]

KONZA (cleanse)konzani akhate...Mat 10:8akhate akonzedwa...Mat 11:5kodi sanakonzedwa khumi...Luk 17:17[onaninso: yeretsa]

KONZA (prepare)inu mumandikonzera chakudya...Mas 23:5konzani njira ya Chauta...Yes 40:3mukakonze mseu woti...Yes 62:10konzani mseu wodzadzeramo...Marko 1:3osakonzedwera kuchita...Luk 12:47ndikupita kukakukonzerani...Yoh 14:2[onaninso: konzekera]

KONZEKERA (prepare)linali tsiku lokonzekera...Yoh 19:14[onaninso: konza]

KONZERA (prepared)malo amene ndakukonzerani...Eks 23:20Chauta wakonza kuti...Zef 1:7amene atatewo adawakonzera...Mat 20:23chimene mudakonza kuti...Luk 2:31natikonzeratu kuti tilandire...Aro 9:23Mulungu adawokonzera amene...1 Akor 2:9ndiye amene adatikonzeratu...2 Akor 5:5iye adatikonzeratu kuti...Aef 2:10iye adawakonzera mzinda...Aheb 11:16[onaninso: sosa]

KONZERA CHIWEMBU (conspire)mukukonzekera kumchitira Chauta chiwembu...Nah 1:9

KOPA (allure)ndidzamkopa ndi...Hos 2:14[onaninso: nyengerera]

KORESI (Cyrus)mfumu ya Peresiya; wonenedwa kukhala wodzodzedwa waMulungu...Yes 44:28-45:1

KORINTO (Corinth)Paulo adagwirako ntchito...Mac 18:1-18malo omwe kunali kachisi...1 Akor 1:2unachezeredwa ndi Apollo...Mac 19:1

KORNELIO (Cornelius)anali munthu wotsata chipembedzo...Mac 10:1-48

KORONA (crown)muika korona wa golidi...Mas 21:3munaipsa korona wake...Mas 89:39koma pa iyeyu korona...Mas 132:18korona wa anzeru...Miy 14:24imvi ndiyo korona wa ulemu...Miy 16:31tsoka kwa korona wakunyada...Yes 28:1adzakhala korona wa ulemerero...Yes 28:5korona wagwa pamutu pathu...Mali 5:16ndipo analuka korona waminga...Mat 27:29iwowa atero kuti alandire korona...1 Akor 9:25chimwemwe changa ndi korona wanga...Afil 4:1wandiikira ine korona wa chilungamo...2 Tim 4:8adzalandira korona wamoyo...Yak 1:12wina angalande korona wako...Chiv 3:11wakukhala naye korona wa golide...Chiv 14:14[onaninso: veka]

KOSALEKEZA (continually)ndidzatsata malamulo anu kosalekeza...Mas 119:44nuyembekeze Mulungu wako kosalekeza...Hos 12:6iyeyu wakhala wansembe kosalekeza...Aheb 7:3[onaninso: nthawizonse]

KOSALEKEZA (endless)kufufuza kosalekeza dongosolo la...1 Tim 1:4[onaninso: wosaonongeka, wosatha]

KOYENERA (decently)zonse zichitike koyenera...1 Akor 14:40

KRETE (Crete)Paulo ayenderako...Mac 27:7-21Tito anasiidwako...Tit 1:5anthu ake oipa ndi aulesi...Tit 1:12

KRISPO (Crispus)wamkulu woyang’anira sunagoge...Mac 18:8anabatizidwa ndi Paulo...1 Akor 1:14

KRUSTALO (Crystal)golidi ndi krustalo sizilingana...Yob 28:17monga mawalidwe a krustalo...Ezek 1:22nyanja ya mandala yonga krustalo...Chiv 4:6

KUBALA ANA (childbearing)adzapulumuka kudzera m’kubala ana...1 Tim 2:15

KUBUULA (groaning)Mulungu anamva kubuula kwao...Eks 2:24

KUBUSA (fields)okhala kubusa ndi kuyang’anira...Luk 2:8[onaninso: minda]

KUBWERA (coming)pa kubwera kwake...1 Akor 15:23

KUCHOTSEDWA (atonement)choipa chimenechi sichidzachosedwa pa inu...Yes 22:14[onaninso: kufafaniza, kuyanjanitsa, mwambo wopepeseramachimo,ombola]

KUDA (black)khungu langa lada...Yob 30:30ndi lakuda ngati khungubwi...Nyi 5:11kapena kulidetsa bii...Mat 5:36kavalo wakuda...Chiv 6:5dzuwa lidada...Chiv 6:12

KUDA (blackness)ndiveka thambo ndi kuda...Yes 50:3

Page 67: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

zimene mdima wakuda bii...Yuda 13

KUDA (dark)wakuda ine...Nyi 1:5nasanduliza usana ude...Amo 5:8ndipo kudzadera inu...Mika 3:6

KUDANDAULA (complaint)lero lomwe kudandaula kwanga...Yob 23:2nditsamila kudandaula kwanga...Mas 142:2[naninso: chifukwa, chitsutsano]

KUDYA (feeds)Efraimu akudya mphepo...Hos 12:1[onaninso: dyetsa]

KUDZALA (fullness)chifukwa mwa kudzala kwake...Yoh 1:16[onaninso: chidzalo, khuta, kudzaza, kwaniridwa,

makwaniridwe]

KUDZAZA (fullness)kufikira kudzaza kwa anthu amitundu...Arom 11:25[onaninso: chidzalo, khuta, kudzala, kwaniridwa,

makwaniridwe]

KUDZICHEPETSA (humble)dzichepetseni pamaso pa Ambuye...Yak 4:10dzichepetseni pamaso pa...1 Pet 5:6[onaninso: odzichepetsa]

KUDZICHEPETSA (humbles)nadzichepetsa apenye...Mas 113:6

KUDZICHEPETSA (humility)ndimkatumikira Ambuye modzichepetsa...Mac 20:19ndi kudzichepetsa mwini wake...Akol 2:18kudzichepetsa, chifatso...Akol 3:12koma nonsenu muvale kudzichepetsa...1 Pet 5:5[onaninso: chifatso, fatsa]

KUDZIKUZA (arrogance)kunyada ndi kudzikuza...Miy 8:13kunyada kwa ozikudza...Yes 13:11

KUDZIKUZA (magnify)ndi kudzikuza koposa milungu...Dan 11:36[onaninso: bukitsa]

KUDZIKUZA (pride)anthu odzikuza andipondereze...Mas 36:11munthu wa mtima wodzikuza...Miy 16:18imachepetsa aliyense wodzikuza...Dan 4:37[onaninso: kudzitama, kudzitukumula, kunyada, nyadira]

KUDZIKUZA (proud)mafunde ako odzikuza...Yob 38:11 lililonse lolankhula modzikuza...Mas 12:3amalanga koopsa anthu odzikuza...Mas 31:23wosasamala wodzikuza...Mas 40:4wooneka wonyada ndi wodzikuza...Mas 101:5koma anthu odzikuza...Mas 138:6wopambana mtima wodzikuza...Mlal 7:8Mulungu amatsatsa odzikuza...1 Pet 5:5[onaninso: dukidwa, kudzitama, nyada]

KUDZILETSA (self-control)za chilungamo, za kudziletsa...Mac 24:25ngati sungathe kudziletsa...1 Akor 7:9kufatsa ndi kudziletsa...Agal 5:23osakhoza kudziletsa...2 Tim 3:3muwonjezerepo kudziletsa...2 Pet 1:6

KUDZITAMA (arrogant)chifukwa cha kudzitama...Yes 10:12

KUDZITAMA (pompous)ankalankhula zodzitama...Dan 7:8

KUDZITAMA (pride)kunyada, kudzitama...Miy 8:13pamene adayamba kudzitama...Dan 5:20[onaninso: kudzikuza, kudzitukumula, kunyada, nyadira]

KUDZITAMA (proud)chomwecho munthu wodzitama...Hab 2:5[onaninso: dukidwa, kudzikuza, nyada]

KUDZITAMANDIRA (rejoicing)ndi kudzitamandira kwa chiyembekezocho...Aheb 3:6[onaninso: chimwemwe, kondwera]

KUDZITUKUMULA (conceit)mtima wodzikonda kapena kudzitukumula...Afil 2:3

KUDZITUKUMULA (conceited)tisakhale odzitukumula...Agal 5:26

KUDZITUKUMULA (pride)kuopa kuti angadzitukumule...1 Tim 3:6[onaninso: kudzikuza, kudzitama, kunyada, nyadira]

KUDZIWA KULANKHULA (eloquent)ine sindidziwa kulankhula bwino...Eks 4:10anali munthu wodziwa kulankhula...Mac 18:24

KUDZOZA (anointing)mafuta opatulika akudzoza nawo...Eks 37:29atamdzoza ndi mafuta...Yak 5:14muli nako kudzoza...1Yoh 2:20kudzoza kumene munalandira...1Yoh 2:27

KUDZULA (plucked)iwo amene anakudzula tsitsi langa...Yes 50:6[onaninso: kolowola, thyola]

KUFAFANIZA (atonement)ndi kufafanizira zonse unazichita...Ezek 16:63[onaninso: kuchotsedwa, kuyanjanitsa, mwambo wopepeseramachimo,ombola]

KUFIKA (coming)chipulumutso chako chifika...Yes 62:11chizindikiro cha kufika kwanu...Mat 24:3

KUFUNKHIDWA (plundering)chifukwa cha kufunkhidwa kwa mwana...Yes 22:4[onaninso: landa]

KUFUULA (singing)lilime lathu linafuula mokondwera...Mas 126:2[onaninso: kuimba]

KUGONJETSA (captivity)ndi kugonjetsa ganizo lonse...2 Akor 10:5[onaninso: ukapolo, undende]

KUGWETSA (casting)ndikugwetsa matsutsano...2 Akor 10:5[onaninso: taya]

KUIMBA (singing)pamaso pake mukuimba...Mas 100:2nthawi yoyimba mbalame...Nyi 2:12ndipo anthu akuimba….Yes 14:7

Page 68: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kukondwa ndi kuimba...Yes 35:2akuimba mosangalala...Yes 35:10[onaninso: kufuula]

KUITANA (calling)mphatso zake ndi kuitana kwake...Aro 11:29[onaninso: maitanidwe]

KUKANGANA (contention)kukangana kudzatha...Miy 22:10munthu wokangana...Yer 15:10ufiti, chidani, kukangana...Agal 5:20[onaninso: mkangano]

KUKHALA MOSAVUTA (ease)amene mumakhala mosavutika...Amo 6:1[onaninso: mtendere, pumula]

KUKHALA WOSALANGIKA (acquit)sadzalola wochimwa akhale wosalangika...Nah 1:3

KUKHOZA (ability)okhoza kuimirira m’chinyumba cha mfumu...Dan 1:4[onaninso: kutha, mphamvu, nzeru]

KUKHOZA (able)ngati ukhoza kuziwerenga zimenezo...Gen. 15:5sadzalola inu kuyesedwa koposa kumene mukhoza...1 Akor10:13Mulungu akhoza...2 Akor 8:9mukakhozetu...Aef 3:18[onaninso: kutha]

KUKOKA (burden)dzombe ndi kukoka miyendo...Mlal 12:5[onaninso: chinthenda, katundu, lemetsa, nkhawa]

KUKOMA MTIMA (favor)kukoma mtima kwanu kuli...Mas 5:12kukoma mtima kwake nkwa moyo onse...Mas 30:5koma kukoma mtima kwake...Miy 19:12[onaninso: chisomo, komera mtima, konda]

KUKONDANA (love)ndiyo nyengo yakukondana...Ezek 16:8koma kukondana ndiko...Aro 13:8[onaninso: chikondano, chikondi, konda, kondana]

KUKONDERA (favoritism)Mulungu sakondera paja...Agal 2:6

KUKONDWERA (gladness)momwemo tsiku lakukondwera inu...Num 10:10tsiku la madyerero ndi kukondwera...Est 9:17adzakhala ndi kusekerera ndi kukondwa...Yes 35:10

KUKONGOLA (beauty)kupenya kukongola kwake...Mas 27:4kukongola kungonyenga...Miy 31:30adzaona mfumu m’kukongola kwake...Yes 33:17alibe maonekedwe, pena kukongola...Yes 53:2[onaninso: chisomo, koma, kongoletsa, ulemelero]

KUKONZA MTEMBO NDI MANKHWALA (embalm)akonze ndi mankhwala mtembo wa bambo ake...Gen 50:2

KUKWATIRA (marrying)ankakwatira ndi ku kwatiwa...Mat 24:38

KUKWERA (depth)kupingasa, ndi utali, ndi kukwera...Aef 3:18[onaninso: kuya]

KULA MSINKHU (full-grown)uchimowo utakula msinkhu...Yak 1:15

KULA (grow)tikakule mzinthu zonse...Aef 4:15koma kulani mchisomo...Aheb 1:11

KULANDA (cheat)pasakhale wina wakulanda inu...Akol 2:8aliyense asakunyengeni ndi kulanda...Akol 2:18[onaninso: nyenga, sautsa]

KULALIKIRA (preaching)ndi kulalika mnyumba ya...Mac 5:42wabwino umene ndimaulalika...Aro 16:25kulalika kwathu nkwachabe...1 Akor 15:14

KULANKHULA-LANKHULA (chatter)kulankhula-lankhula kungopatsa umphawi...Miy 14:23

KULANKHULA MOCHENJERA (flatter)sindidziwa kulankhula mochenjera...Yob 32:22[onaninso: syasyalika]

KULEDZERA (drunkenness)udzadzala ndi kuledzera ndi chisoni...Ezek 23:33ndi maphwando, kuledzera...Luk 21:34pasakhale dyera kapena kuledzera...Aro 13:13dumbo, kuledzera...Agal 5:21zilakolako zoipa, kuledzera...1 Pet 4:3[onaninso: zandiritsa]

KULEMERA (weight)kulemera koposa kwakukulu...2 Akor 4:17[onaninso: cholemetsa, miyeso, miyeso]

KULEZA MTIMA (longsuffering)chimwemwe, mtendere, kuleza mtima...Agal 5:22Yesu Khristu akaonetsere kuleza mtima...1 Tim 1:16kuleza mtima kwa Mulungu kumalindira...1 Pet 3:20[onaninso: chipiriro, kusapsa mtima msanga]

KULEZA MTIMA (patience)ndakupembani, lezerani mtima...Mat 18:26[onaninso: chipiriro, kupirira]

KULIMBANA (conflicts)kunjako zolimbana...2 Akor 7:5

KULIMBIKA (boldness)ndilimbika mtima kwambiri...2 Akor 7:4ndi chiyandikiro cholimbika cha...Aef 3:12komatu mwa kulimbika mtima konse...Afil 1:20ndi kulimbika kwakukuru...1 Tim 3:13kuti tikhale nako kulimbika mtima...1 Yoh 4:17[onaninso: chilimbikitso]

KULIMBIKA MTIMA (confidence)ngati tigwiritsa kulimbika mtima...Aheb 3:6tikakhale nako kulimbika mtima...1 Yoh 2:28[onaninso: khulupirira]

KULINDIRA (expectation)koma kulindira kwina koopsa kwa chiweruzo...Aheb 10:27[onaninso: chiyembekezo]

KULINDIRA (waiting)anali kulindira matonthozedwe a Israyeli...Luk 2:25[onaninso: dikira, yembekezera]

KULINGANA (equality)potero padzakhala kulingana...2 Akor 8:14

Page 69: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KULIRA (crying)kapena kulira, kapena chowawitsa...Chiv 21:4[onaninso: fuula]

KULIRA MOKUWA (mourn)moyo wako udzalira chokuwa...Miy 5:11)nthawi yolira maliro...Mlal 3:4lirani, lirani misozi...Yak 4:9pa dziko lapansi adzamlira...Chiv 1:7[onaninso: chisoni]

KULIRA (mourning)kanani zitaona kulira...Gen 50:11ndimayenda woliralira...Mas 38:6choncho masiku ako olira...Yes 60:20chakudya munthu wolira...Yer 16:7kulira kwao kuja...Yer 31:13kulira maliro ku Yerusalemu...Zekariya 12:11chisoni, lirani misozi...Yak 4:9

KULIRA (sorrow)akulilira msonkhano woikika...Zef 3:18[onaninso: chisoni, mantha, kupweteka, kusauka]

KULITSA (enlarges)wakukulitsa chikhumbo chake...Hab 2:5[onaninso: kuza]

KULITSIDWA (exalted)akulitsidwe Mulungu wa...1 Sam 22:47[onaninso: kwezeka, kuzika]

KULOSA (divination)kudzadela inu opanda kulosa...Mik 3:6[onaninso: mlauli, mbwebwe,ombeza]

KULU (abundant)monga mwa chifundo chake chachikulu...1 Pet 1:3[onaninso: chuluka, dzala]

KULU (deep)tulo tatikulu ndipo anagona...Gen 2:21[onaninso: bi, kuya, zama]

KULU (high)wansembe wa Mulungu wamkulukulu...Gen 14:18mkulu wa ansembe wokhulupirika...Aheb 2:17[onaninso: mwamba]

KUM’MAWA (east)wakuyenda cha kum’mawa...Gen 2:14mphepo ya kum’mawa...Eks 10:13pomwazikira mphepo ya kum’mawa...Yob 38:24monga kum’mawa kutanimpha...Mas 103:12mbeu zako kuchokera kum’mawa...Yes 43:5anzeru akum’mawa anafika...Mat 2:1kuti ambiri a kum’mawa ndi...Mat 8:11anthu adzachokera kum’mawa...Luk 13:29

KUMANA (meet)konzekerani kuti mukumane ndi...Amo 4:12tulukani kukakomana naye...Mat 25:6kukakumana ndi Ambuye...1 Ates 4:17[onaninso: kumika]

KUMANA (meeting)m’chihema chokomanako...Eks 27:21

KUMASULIRA ( interpretations)Kodi mwini kumasulira si Iye...Gen 40:8ndi kundidziwitsa kumasulira kwake...Dan 5:16

KUMBUKIRA (remember)komabe udzandikumbuke...Gen 40:14uzikumbukira tsiku la sabata...Eks 20:8kumbukirani kuti mudaali...Deut 15:15muzikumbukira ntchito zodabwitsa...1 Mbir 16:12musakumbukire machimo a unyamata...Mas 25:7ndimakukumbukirani usiku...Mas 119:55uzikumbukanso mlengi wako...Mlal 12:1musakumbukire zakale...Yes 43:18ndikukukumbukirani mmene...Yer 2:2sindidzakumbukiranso machimo aowo...Yer 31:34osakumbukira pangano lachibale...Amo 1:9pa mkwiyo mukumbukire chifundo...Hab 3:2wakumbukira chipangano chake...Luk 1:72kumbukirani za mkazi wa Loti...Luk 17:32kumbukirani mau aja a Ambuye...Mac 20:35kumbukirani kuti ndili m’maunyolo...Akol 4:18kumbukira Yesu Khristu...2 Tim 2:8mudzikumbukira atsogoleri anu...Aheb 13:7[onaninso: tchula]

KUMBUKIRA (remembered)Mulungu adakumbukira Nowa...Gen 8:1nakumbukira chipangano chake...Eks 2:24akumbukira chipangano chake chosatha...Mas 105:8ndinakumbukira maweruzo anu...Mas 119:52adatikumbukira pamene adani...Mas 136:23nkumalira tikukumbukira Ziyoni...Mas 137:1amene adamkumbukira wosaukayo...Mlal 9:15adakumbuka za makedzana...Yes 63:11Petro adakumbukira mau aja...Mat 26:75ndidakumbukira mau aja...Mac 11:16

KUMBUKIRA (remembrance)pakuti muimfa m’mosakumbukira inu...Mas 6:5ndikumbukira nyimbo yanga usiku...Mas 77:6zakale sizikumbukika ...Mlal 1:11mundikumbutse zakale...Yes 43:26zimenezi kuti muzindikumbukira...Luk 22:19zimenezi kuti muzindikumbukira...1 Akor 11:24

KUMBUKIRA (thinks)koma Ambuye andikumbukira ine...Mas 40:17[onaninso: ganiza, yesa]

KUMIKA (awake)maso anga anakumika...Mas 119:148[onaninso: dikira, galamuka, khala maso, uka]

KUMIKA (meet)pakuti mumkumika iye pa...Mas 21:3[onaninso: kumana]

KUMVA (listen)chifukwa simungathe kumva mau...Yoh 8:43nachita misala, mukumva iye...Yoh 10:20[onaninso: mvera]

KUMVA ZOWAWA (suffer)Khristu amve zowawa...Luk 24:46ife timva zowawa...Aro 8:17chimodzi chimva zowawa...1 Akor 12:26komatunso kumva zowawa...Afil 1:29m’menemo ndimva zowawa...2 Tim 2:9ndi kumvako zowawa...1 Pet 2:20kumva zowawa chifukwa...1 Pet 3:17asamve zowawa wina...1 Pet 4:15uti udzamve zowawa...Chiv 2:10[onaninso: phwetekwa, zunzidwa]

KUMVA ZOWAWA (suffered)Khristu kumva zowawa...Luk 24:26

Page 70: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mudamva zowawa zambiri...Agal 3:4adamva chowawa kunja kwa chipata...Aheb 13:12pakutinso Khristu anamva zowawa...1 Pet 2:21Khristunso anamva zowawa kamodzi...1 Pet 3:18Khristu adamva zowawa m’thupi...1 Pet 4:1mutamva zowawa kanthawi...1 Pet 5:10[onaninso: tayikitsa]

KUMVERA (obedience)yonse kumkhulupirira ndi kumvera...Aro 1:5chifukwa cha kumvera munthu...Aro 5:19ganizo lonse ku kumvera kwa Khristu...2 Akor 10:5pokhulupirira kumvera kwako...Fil 21adaphunzira kumvera pakumva...Aheb 5:8kuti mumvere Yesu Khristu...1 Pet 1:2

KUMVERA (obedient)ngati muli okonzeka kundimvera...Yes 1:19ambirimbiri ankamvera...Mac 6:7anthu amitundu ina kumvera...Aro 15:18a pansi pano muziwamvera...Aef 6:5adakhala womvera kufikira...Afil 2:8ndi omvera amuna ao...Tit 2:5muzikhala ngati ana omvera...1 Pet 1:14

KUMVERA (understanding)wadzipemphera nzeru zakumvera milandu...1 Maf 3:11[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kuzindikira, luntha, luso,mvetsa, nzeru]

KUMVETSA (comprehend)zimene sitingathe kumvetsa...Yob 37:5[onaninso: zindikira]

KUMWAMBA (above)za m’thambo la kumwamba...Eks 20:4kuchokera kumwamba...2 Sam 22:17iye wochokera kumwamba...Yoh 3:31ine ndine wochokera kumwamba...Yoh 8:23kwa inu kuchokera kumwamba...Yoh 19:11funani za kumwamba...Akol 3:1zichokera kumwamba...Yak 1:17mbalame za kumwamba...Luk 9:58[onaninso: m’mwamba, pamwamba, posa]

KUMWAMBA (air)ndi mbalame zakumwamba zisa...Luk 9:58[onaninso: mlengalenga]

KUMWAMBA (heaven)analitcha thambolo kumwamba...Gen 1:8Chauta kumwambako wawerama...Mas 14:2ngokhazikika kumwambako...Mas 119:89paja Mulungu ali kumwamba...Mlal 5:2thambo la m’mwamba ndiye...Yes 66:1munthu wotha kupima zakumwamba...Yer 31:37ufumu wakumwamba wayandikira...Mat 3:2Atate wanu wa kumwamba...Mat 5:16monga kumwamba chomwecho...Mat 6:10chizindikiro chochokera kumwamba...Marko 8:11ndinachimwira kumwamba ndi...Luk 15:18kulibe munthu anakwera kumwamba...Yoh 3:13anakupatsani mkate wa kumwamba...Yoh 6:32adadza mau ochokera kumwamba...Yoh 12:28ndi kutsika kumwamba...Mac 11:5ndipo m’mwamba munatsika mvula...Yak 5:18onse kumwamba angoti chete...Chiv 8:1

KUMWAMBA (heavenly)inunso Atate wanu wa kumwamba...Mat 6:14ambirimbiri a gulu la kumwamba...Luk 2:13ngati ndikuuzani za kumwamba... Yoh 3:12

monga wakumwamba, ateronso akumwamba...1 Akor15:48dalitso la mzimu m’za kumwamba...Aef 1:3nalawa mphatso ya kumwamba...Aheb 6:4koma zam’mwamba zenizeni ziyeretsedwe...Aheb 9:23lina loposa ndilo la m’Mwamba...Aheb 11:16Yerusalemu wa kumwamba...Aheb 12:22

KUMWAMBA (heavens)kumwamba ndi zonse zili kumeneko...Deut 10:14onani kumwamba ndi kumwamba...1 Maf 8:27Chauta ndiye adalenga zakumwamba...1 Mbir 16:26zakumwamba zinalalikira...Mas 19:1zakumwamba zionetsera ulemerero...Mas 50:6zakumwamba ndi zanu...Mas 89:11ankakhazikitsa zakumwamba...Miy 8:27[onaninso: miyamba, mlengalenga, thambo]

KUNJA (outward)ndi maonekedwe akunja...1 Pet 3:3

KUNJENJEMERA (terror)koma kunawagwera kunjenjemera...Dan 10:7[onaninso: choopsa, mantha, opsa]

KUNSI (depths)moyo wanga kunsi kwa manda...Mas 86:13[onaninso: kuya, zama]

KUNYADA (pride)amavala kunyada ngati mkanda...Mas 73:6kunyada, kudzitama...Miy 8:13kunyada kwa munthu...Miy 29:23[onaninso: kudzikuza, kudzitama, kudzitukumula, nyadira]

KUNYOZA (contempt)wamphulupulu padzanso kunyoza...Miy 18:3[onaninso: kuyesedwa chabe, mnyozo]

KUOMBOLEDWA (deliverance)ena anakwapulidwa osalola kuomboledwa...Aheb 11:35[onaninso: chipulumutso]

KUONEKA (countenance)kuoneka kwake kunali ngati...Mat 28:3[onaninso: maonekedwe, nkhope]

KUOPA (fearing)ndiye wodzipereka kukuopani...Mas 119:38kumodzi, akuopa Ambuye...Akol 3:22[onaninso: opa]

KUOPSA (fierceness)kuopsa kwako, kunyada...Yer 49:16[onaninso: ukali]

KUPEMBEDZA (religion)amalamula anthu zambiri pa za kupembedza...Akol 2:23[onaninso: chipembedzero, mapembedzedwe, wopembedza]

KUPEMBEDZA MAFANO (idolatre)pewani kupembedza mafano...1 Akor 10:14kupembedza mafano, ufiti...Agal 5:10

KUPERA (grinding)potsika mau akupera...Mlal 12:4ndi kupera nkhope ya wosauka...Yes 3:15awiri adzakhala opera...Mat 24:41

KUPHUNZIRA (learning)naonjezere kuphunzira...Miy 1:5[onaninso: kutilangiza, kuwerengetsa]

Page 71: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KUPIRIRA (patience)nabala zipatso ndi kupirira...Luk 8:15[onaninso: chipiriro, kuleza mtima]

KUPRO (Cyprus)ananenedwa m’mauneneri...Num 24:24;Yes 23:1-12;Yer 2:10Akhristu analalikira kwa Ayuda a kumeneko...Mac 11:19,20Paulo ndi Barnaba anachezako...Mac. 13:4-13; 15:39

KUPUSA (foolishness)Inu Mulungu, mudziwa kupusa...Mas 69:5amaonetsa poyera kupusa...Miy 12:23kupusa kwake kwa munthu...Miy 19:3kupusa kumakhala mumtima...Miy 22:15chimene chimaoneka ngati kupusa...1 Akor 1:25[onaninso: chibwana, opusa, zopusa]

KUPWETEKA (sorrow)chifukwa chake chotsani zopweteka m’mtima mwako...Mlal

11:10kupweteka kwako kuli kosapola...Yer 30:18[onaninso: chisoni, mantha, kulira, kusauka]

KURENE (Cyrene)mzinda wa Chigriki kum’mawa kwa Africakwawo kwa Simoni wolandira Yesu mtanda...Mat 27:32kunali sunagoge...Mac 6:9Akhristu ochokera kumeneku anakhala ma mishonale...Mac11:20

KURU (great)anachitira choipa ichi chachikuru...1 Sam 6:9Yehova ali wamkuru...1 Mbir 16:25nyumba nditi ndimangeyi ndiyayikuru...2 Mbir 2:5amene achita zazikuru ndi...Yob 5:9Akuru sindiwo eni nzeru...Yob 32:9la inu munsonkhano waukuru...Mas 22:25ntchito zanu nzazikuru...Mas 92:5Inu wamkurukuru...Mas 104:1Yehova anawachitira iwo zazikuru...Mas 126:2ngakhale kuima m’malo mwa akuru...Miy 25:6wa m’kati mwako ali wamkuru...Yes 12:6udzifunira wekha zinthu zazikuru...Yer 45:5tsiku lalikuru la Yehova...Zef 1:14adzatchulidwa wamkuru ku...Mat 5:19akafuna kukhala wamkuru mwa inu...Mat 20:26madontho akuru a mwazi...Luk 22:44kuti iye yekha ndiye munthu wamkuru...Mac 8:9wamkuru ndi Artemi wa ku...Mac 19:28ndagwidwa ndi chisoni chachikuru...Aro 9:2kuchitira Mulungu ulemu nchachikuru...1 Tim 3:16chipindulitsa kwakukuru...1 Tim 6:6koma m’nyumba yayikuru simuli...2 Tim 2:20ulemerero wa Mulungu wamkuru...Tit 2:13ndipo lidzikuzira zazikuru...Yak 3:5mafumu a dziko ndi akuru...Chiv 6:15Babulo wamkuru...Chiv 17:5mpando wachifumu waukuru woyera...Chiv 20:11akufa, akuru ndi ang’ono...Chiv 20:12

KUSABALA (barren)analibe ana chifukwa anali wosabala...Gen 11:30amapatsa banja mkazi wosabala...Mas 113:9azimai osabala...Luk 23:29chumba iwe osabala...Agal 4:27[onaninso: chumba, opanda zipatso, uma, wosabala mwana]

KUSADZIWA (ignorance)kuti munachita mosadziwa...Mac 3:17nthawi za kusadziwako tsono...Mac 17:30kulankhula kosadziwa kwa anthu...1 Pet 2:15[onaninso: kusazindikira]

KUSADZIWA (ignorant)wamthengo, wosadziwa kanthu...Mas 73:22Abrahamu satidziwa ife...Yes 63:16sindifuna kuti mukhale osadziwa...1 Akor 12:1ngati wina akhala wosadziwa...1 Akor 14:38chifundo ndi osadziwa ndi olakwa...Aheb 5:2

KUSAKAZA-KWA MSANGA KUFUNKHA-KOFULUMIRA(Maher-shalal-hash-baz)

dzina latanthauzo la chizindikiro la mwana wamwamuna wachiwiri wa YesayaUneneri wa kugwa kwa Damasiko ndi Samariya...Yes 8:1-4

KUSAMVERA (disobedience)chifukwa cha kusamvera kwa...Aro 5:19mwa ana a kusamvera...Aef 2:2cholakwira chirichonse ndi chosamvera...Aheb 2:2

KUSANI-RISATAIMU (Cushan-Rishathaim)mfumu ya ku Mesopotamiya; inazunza Israeli...Ower 3:8Otiniyeli anaombola Yuda kuchokera kwa iye...Ower 3:9

KUSAPSA MTIMA MSANGA (longsuffering)wosapsa mtima msanga...Mas 86:15[onaninso: chipiriro, kuleza mtima]

KUSAUKA (anguish)kusaukako chifukwa...Yoh 16:21[onaninso: chipsinjo, kusautsika, kuwawa mtima, nkhawa]

KUSAUKA (poverty)kusauka kwao kwenikweni...2 Akor 8:2[onaninso: umphawi]

KUSAUKA (sorrow)ndidzachulukitsa kusauka kwako ndi potenga mimba...Gen 3:16[onaninso: chisoni, mantha, kulira, kupweteka]

KUSAUTSIKA (anguish)kusautsika ndi...Mas 119:143[onaninso: chipsinjo, kusauka, kuwawa mtima, nkhawa]

KUSAWERUZIKA (lawlessness)inu akuchita kusaweruzika...Mat 7:23avumbulutsidwa wosaweruzikayo...2 Ates 2:8[onaninso: kusayeruzika]

KUSAYERUZIKA (lawlessness)wakuchita tchimo achitanso kusayeruzika...1 Yoh 3:4[onaninso: kusaweruzika]

KUSAZINDIKIRA (ignorance)ochita anthu mosazindikira...Aheb 9:7[onaninso: kusazindikira]

KUSEKA (laughter)pakamwa pathu panadzala ndi kuseka...Mas 126:2kuseka kwanu kusanduke kulira...Yak 4:9

KUSHASHALIKA (flattering)pakamwa poshashalika mpoononga...Miy 26:28mau okoma ndi oshashalika...Aro 16:18kwanuko ndi mau oshashalika...1 Ates 2:5amangotama anthu moshashalika...Yuda 16

KUSI (Cush)mwana wamwamuna wamkuru wa Hamu...1 Mbir 1:8-10— dzina lina la Etiopia...Yes 18:1

KUSINZA (drowsiness)

Page 72: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kusinza kudzaveka munthu sanza...Miy 23:21

KUSIYANA (factions)pakhale kusiyana maganizo...1 Akor 11:19

KUSONKHANA (gathering)kusonkhana kwa maziko...Gen 1:10kusonkhana pamodzi kwathu kwa iye...2 Ates 2:1

KUSONKHANA PAMODZI (assembling)osaleka kusonkhana kwathu pamodzi...Aheb 10:25

KUSYA (cassia)nza mure, khonje ndi kusya...Mas 45:8

KUTA (cover)amene mudzikuta nako kuunika...Mas 104:2[onaninso: phimba, vundikira]

KUTA (covered)mudzakuta ndi mtambo...Mali 3:44[onaninso: kwirira, phimba]

KUTALI (far)kuchokera kutali...Yes 60:4kwa onse a kutali...Mac 2:39amene munali kutali...Aef 2:17[onaninso: patali]

KUTHA (ability)adapereka monga adathera...2 Akor 8:3[onaninso: kukhoza, mphamvu, nzeru]

KUTHA (able)pakuti akutha ndani kuweruza...1 Maf 3:9Chauta angathe kukupatsani zambiri...2 Mbir 25:9Mulungu amene timamtumikira ife angathe...Dan 3:17Mulungu angathe kusandulitsa miyala ili apayi...Mat 3:9mukukhulupirira kuti ndingathe kuchita zimenezi...Mat 9:28muziopa amene angathe kuononga thupi ndi mzimu...Mat10:28kodi inu mungathe kumwa nao chikho...Mat 20:22iyeyo angathe...2 Tim 1:12ndipo sangathe...2 Tim 3:7ndiye kuti angathe...Aheb 2:18tsono tingathe...Aheb 11:19iye amene angathe...Yuda 24ndipo angathe...Chiv 6:17[onaninso: kukhoza]

KUTHA MPHAMVU (feeble)adachirikiza munthu wotha mphamvu...Yob 4:4[onaninso: fooka, lefuka, onda]

KUTHAMANGA (race)chiphona kuthamanga mnjira...Mas 19:5athamanga msanga sapambana liwiro...Mlal 9:11tithamange ndi khama mpikisano...Aheb 12:1[onaninso: mpikisano wa liwiro]

KUTHWA (sharp)lupanga lakuthwa...Miy 5:4

KUTHYOKA (affliction)chisoni ndi kuthyoka kwa Yosefe...Amo 6:6[onaninso: chisautso, kuzunza, kuzunzika, masautso, mazunzo,nsauko, nthenda]

KUTILANGIZA (learning)zinalembedwa kutilangiza...Aro 15:4[onaninso: kuphunzira, kuwerengetsa]

KUTSUTSANA (dispute)adayamba kutsutsana...Luk 22:24

KUUNIKA (light)kuunika kwa oipa kudzazima...Yob 18:5kuunika kudzawala pa njira...Yob 22:28kuunika kwa oipa kuletsedwa...Yob 38:15weramutsani ife kuunika...Mas 4:6Yehova ndiye kuunika kwanga...Mas 27:1tumizani kuunika kwanu...Mas 43:3kuunika kufesekera olungama...Mas 97:11ndi kuunika kwa panjira...Mas 119:105kuunika kwa olungama...Miy 13:9kuunika kwa maso kukondweretsa...Miy 15:30indetu kuunika nkokoma...Mlal 11:7kuunika kwake kudzawalitsa...Yes 58:8pakuti kuunika kwako kwafika...Yes 60:1Yehova adzakhala kuunika kwako...Yes 60:20anga atuluka ngati kuunika...Hos 6:5ndinu kuunika kwa dziko lapansi...Mat 5:14muwalitse inu kuunika kwanu...Mat 5:16mbadwo wao koposa ana akuunika...Luk 16:8ndi moyowu unali kuunika...Yoh 1:4uku ndiko kuunika kwenikweni...Yoh 1:9kuunika kunadza ku dziko lapansi...Yoh 3:19kuchita zoipa adana nako kuunika...Yoh 3:20wochita choonadi adza kukuunika...Yoh 3:21Ine ndine kuunika kwa dziko...Yoh 8:12khulupirirani kuunikako...Yoh 12:36ndadza Ine kuunika ku dziko...Yoh 12:46kuunika kudzawala kutuluka...2 Akor 4:6koma tsopano muli kuunika...Aef 5:8inu nonse muli ana a kuunika...1 Ates 5:5mulowe kuunika kwake...1 Pet 2:9kuti Mulungu ndiye kuunika...1 Yoh 1:5m’kuunika monga iye ali mkuunika...1 Yoh 1:7amene anena kuti ali m’kuunika...1 Yoh 2:9ndipo sasowa kuunika kwa nyali...Chiv 22:5[onaninso: kuwala, unikira]

KUWABATIZA (baptizing)kuwabatiza iwo...Mat 28:19kudzabatiza ndi madzi...Yoh 1:31

KUWALA (light)tiyeni tiyende nkuwala...Yes 2:5kuwala kwake kwa mwezi...Yes 30:26[onaninso: kuunika, unikira]

KUWAWA MTIMA (anguish)kuwawa mtima kwandigwera...2 Sam 1:9nsautso ndi kuwawa mtima...Aro 2:9mchisautso chambiri ndi kuwawa mtima...2 Akor 2:4[onaninso: chipsinjo, kusauka, kusautsika, nkhawa]

KUWERENGETSA (learning)kuwerengetsa kwako kwakuchititsa misala...Mac 26:24[onaninso: kuphunzira, kutilangiza]

KUYA (deep)amakundika zakuya mosungiramo...Mas 33:7madzi akuya aitanizana...Mas 42:7kupitirira mwa kuya...Yes 63:13madzi akuya anandizungulira...Yon 2:5madzi akuya anamveketsa mau...Habak 3:10kankhira kwa kuya...Luk 5:4ndinakhala m’kuya tsiku...2 Akor 11:25[onaninso: bi, kulu, zama]

KUYA (depth)sizinakhala nalo dothi lakuya...Mat 13:5ngakhale utali, ngakhale kuya...Aro 8:39

Page 73: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kuya kwake kwa kulemera...Aro 11:33[onaninso: kukwera]

KUYA (depths)zonse m’nyanja yakuya...Mika 7:19amene sanazindikira zakuya za satana...Chiv 2:24[onaninso: kunsi, zama]

KUYANJANITSA (atonement)ndidzakuyanjanitsani ndi chiyani...2 Sam 21:3[onaninso: kuchotsedwa, kufafaniza, mwambo wopepeseramachimo,ombola]

KUYESEDWA CHABE (contempt)zambiri ndi kuyesedwa chabe...Marko 9:12[onaninso: kunyoza, mnyozo]

KUVINA (dancing)mwana wang’ombeyo ndi kuvinako...Eks 32:19anamva kuyimba ndi kuvina...Luk 15:25[onaninso: chikondwerero]

KUZA (enlarges)amakuza mitundu ina ya anthu...Yob 12:23[onaninso: kulitsa]

KUZA (exaltation)kukuzaku sikuchokera kum’mawa...Mas 75:6[onaninso: ukulu]

KUZA (exalts)chilungamo chikuza mtundu...Miy 14:34nadzikuza pa zonse zotchedwa...2 Ates 2:4[onaninso: kweza]

KUZA (boast)asadzikuze ngati wakuvulayo...1 Maf 20:11[onaninso: nyada, nyadira]

KUZA (boastful)ndinkachita nsanje ndi anthu odzikuza... Mas 73:3[onaninso: nyada, nyadira]

KUZAZA (wrath)ndi kuzaza kwanu kudzatentha...Mas 89:46[onaninso: kwiya, mkwiyo, udani, ukali]

KUZIDWA (magnified)dzina lanu likulitsidwe ku nthawi...2 Sam 7:26munakuzitsa mau anu koposa...Mas 138:2ndipo dzina la Yesu linakuzidwa...Mac 19:17tsopanonso Khristu adzakuzidwa...Afil 1:20[onaninso: buka]

KUZIKA (exalted)lokuzika loposa...Neh 9:5[onaninso: kulitsidwa, kwezeka]

KUZINDIKIRA (understanding)mpweya wa Wamphamvuyonse wawazindikiritsa...Yob 32:8mundizindikiritse ndipo ndidzasunga...Mas 119:34malangizo anu andizindikiritsa...Mas 119:104mtima wako ku kukuzindikira...Miy 2:2koma masewero a wozindikira...Miy 10:23koma wosauka wozindikira aululitsa zake...Miy 28:11wanzeru ndi wakuzindikira...Yes 11:2[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kumvera, luntha, luso,mvetsa, nzeru]

KUZUNZA (affliction)masiku akuzunza andigwira...Yob 30:16[onaninso: chisautso, kuthyoka, kuzunzika, masautso, mazunzo,

nsauko, nthenda]

KUZUNZIKA (affliction)muyang’ane kuzunzika...1 Sam 1:11anapenya kuti kuzunzika kwao...2 Maf 14:26omangika ndi kuzunzika ndi...Mas 107:10chitonthozo changa m’kuzunzika...Mas 119:50[onaninso: chisautso, kuthyoka, kuzunza, masautso, mazunzo,nsauko, nthenda]

KWANA (enough)zimene siziti “takwana”...Miy 30:15chakwanira, yafika nthawi...Marko 14:41amene ali ndi chakudya chokwanira...Luk 1:17

KWANIRA (accomplished)lembo likwaniridwe...Yoh 19:28[onaninso: chita, chitidwa, kwaniritsidwa]

KWANIRA (content)zindikwanire ziri zonse ndili nazo...Afil 4:11zimenezi zitikwanire...1 Tim 6:8zimene muli nazo zikukwanireni...Aheb 13:5[onaninso: khutira]

KWANIRA (fulfilled)nthawi zao za anthu akunja zakwanira...Luk 21:24chilamulo chikwaniridwe mwa ife...Aro 8:4[onaninso: chitidwa, kwaniritsa, kwaniritsidwa]

KWANIRIDWA (fullness)koma pokwaniridwa nthawi...Agal 4:4a makwaniridwe a nyengozo...Aef 1:10[onaninso: chidzalo, khuta, kudzala, kudzaza, makwaniridwe]

KWANIRITSA (fulfill)Yehova akwaniritse mapempho ako...Mas 20:5kuyenera ife kukwaniritsa chilungamo...Mat 3:15kwaniritsani chimwemwe changa...Afil 2:2nakwaniritse chonkomera chonse...2 Ates 1:11ngati muchita chikwanirire lamulo...Yak 2:8

KWANIRITSA (fulfilled)akondana ndi mnzake wakwaniritsa lamulo...Aro 13:8mau amodzi akwaniritsa lamulo...Agal 5:14[onaninso: chitidwa, kwanira, kwaniritsidwa]

KWANIRITSIDWA (accomplished)chiyenera kukwaniritsidwa...Luk 22:37[onaninso: chita, chitidwa, kwanira]

KWANIRITSIDWA (fulfilled)ziyenera kukwaniritsidwa zonse...Luk 24:44[onaninso: chitidwa, kwanira, kwaniritsa]

KWANITSA (fulfilment)chikondanocho chiri chokwanitsa lamulo...Aro 13:10[onaninso: chitidwa]

KWAPULA (beaten)ndipo adzakukwapulani...Marko 13:9[onaninso: bwanyulidwa, kwapulidwa, menyedwa]

KWAPULA (punish)azitenga munthuyo ndi kumkwapula...Deut 22:18ngakhale kukwapula akulu...Miy 17:26[onaninso: langa]

KWAPULIDWA (beaten)adzakwapulidwa mikwapulo yambiri...Luk 12:47[onaninso: bwanyulidwa, kwapula, menyedwa]

Page 74: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

KWATIRA (married)koma munthu wokwatira...1 Akor 7:33[onaninso: kwatiwa]

KWATIRA (marry)ndi bwino tsono kusakwatira...Mat 19:10nkwabwino kukwatira koposa...1 Akor 7:9[onaninso: kwatiwa, ukwati]

KWATIWA (married)sakwatira kapena kukwatiwa...Mat 22:30mkazi wosakwatiwa...1 Akor 7:34[onaninso: kwatira]

KWATIWA (marry)sakwatira kapena kukwatiwa...Mat 22:30nditi akwatiwe amasiye...1 Tim 5:14[onaninso: kwatira, ukwati]

KWATULA (catches)ndipo mmbulu uzikwatula...Yoh 10:12[onaninso: gwira]

KWATULA (caught)Mzimu wa Ambuye anakwatula Filipo...Mac 8:39[onaninso: gwira, kwatulidwa]

KWATULIDWA (caught)ndipo anakwatulidwa mwana wake...Chiv 12:5[onaninso: gwira, kwatula]

KWAWA (creep)mwa iwo akhala akukwawira...2 Tim 3:6[onaninso: turuka]

KWAWA (creeping)ng’ombe, ndi zokwawa...Gen 1:24maonekedwe ali onse a zokwawa...Ezek 8:10

KWAWA (crept)anakwawira m’tseri...Yuda 4

KWERA (ascend)adzakwera ndani mphiri...Mas 24:3ndikakwera kunka...Mas 139:8ndidzakwera kumwamba...Yes 14:13ukwera pamwamba...Obad 4ali kukwera kumene anali...Yoh 6:62

KWERA (ascended)munakwera pamwamba...Mas 68:18ndani anakwera kumwamba...Miy 30:4munthu anakwera kumwamba...Yoh 3:13m’mene anakwera kumwamba...Aef 4:8yemweyonso anakwera...Aef 4:10ndipo anakwera kunka kumwamba...Chiv 11:12

KWERA (ascending)amithenga a Mulungu anali kukwera ...Gen 28:12Angelo a Mulungu akwera...Yoh 1:51

KWERA (climb)adzakwera pa miyala...Yer 4:29akwera linga ngati anthu ankhondo...Yow 2:7angakhale akwera kumwamba...Amo 9:2koma akwerera kwina...Yoh 10:1

KWEZA (exalt)nadzakweza nyanga ya wodzozedwa...1 Sam 2:10tikweze dzina lake pamodzi...Mas 34:3mkwezeni Yehova Mulungu...Mas 99:5Mulungu wanga, ndidzakukwezeni...Mas 118:28

kumwamba, ndidzakweza mpando...Yes 14:13kweza chopepuka...Ezek 21:26pamene Mulungu amkweza...Yak 1:9[onaninso: lemekeza, sankha]

KWEZA (exalts)chonse chimene chizikweza...2 Akor 10:5[onaninso: kuza]

KWEZA (extol)ndidzakukwezani, Yehova...Mas 30:1kwezani nyimbo yotamanda...Mas 68:4

KWEZA (lift)ndidzakweza manja anga...Mas 63:4ndikweza maso anga kumapiri...Mas 121:1kweza mau ako ngati...Yes 58:1Ambuye, ndipo adzakukwezani...Yak 4:10[onaninso: tukula]

KWEZA (lifted)ndidzakukwezani Yehova...Mas 30:1popeza mtima wako wadzikweza...Ezek 28:2ndipo m’hade anakweza maso...Luk 16:23Mose anakweza njoka m’chipululu...Yoh 3:14m’mene ndikakwezedwa ...Yoh 12:32munthu ayenera kukwezedwa...Yoh 12:34

KWEZA (lofty)mbadwo wokwezatu maso...Miy 30:13[onaninso: kwezeka, tukulidwa]

KWEZEDWA (extolled)adzakwezedwa ndi kutukulidwa...Yes 52:13

KWEZEKA (delight)ndi mtima wake unakwezeka...2 Mbir 17:6[onaninso: chikondwerero, kondwera, sekeretsa]

KWEZEKA (exalted)za olungama zidzakwezeka...Mas 75:10nyanga yathu idzakwezeka...Mas 89:17ndinu wokwezeka kwakukulu...Mas 97:9dzina lake lokha ndi lokwezeka...Mas 148:13ndikudzikweza kwa anthu...Yes 2:11amene Mulungu anamkweza ndi...Mac 5:31kuti ndingakwezeke koposa...2 Akor 12:7Mulungu anamkwezetsa...Afil 2:9[onaninso: kulitsidwa, kuzika]

KWEZEKA (lofty)maso anga sanakwezeka...Mas 131:1[onaninso: kweza, tukulidwa]

KWIRIRA (covered)ngati ndakwirira zolakwa...Yob 31:33wokwiriridwa choipa...Mas 32:1[onaninso: kuta, phimba]

KWIYA (anger)kodi mudzakhala chikwiyire...Mas 85:5wosakwiya msanga...Mas 103:8usamafulumira kukwiya...Mlal 7:9iwe ndi kukwiya...Yer 3:12[onaninso: mkwiyo]

KWIYA (angry)kodi wakwiyiranji...Gen 4:6ndipo anati, asakukwiyiretu Ambuye...Gen 18:30kuwopa kuti angakukwiyireni...Mas 2:12ndiye Mulungu wakwiya...Mas 7:11kodi mudzakhalabe wokwiya...Mas 79:5

Page 75: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

munthu wokwiya msanga...Miy 22:24losinjirira likwiyitsa...Miy 25:23mwamuna wamkwiyo...Miy 29:22usamafulumira kukwiya...Mlal 7:9ndidzawakwiyira anthu anga...Yes 47:6kapena kuwakwiyira...Yes 57:16ndidawakwiyira chifukwa...Yes 57:17wachita bwino pokwiya...Yon 4:4Chauta adaakwiyira...Zek 1:2ndawakwiyira kwambiri...Zek 1:15yense wokwiyira mbale wake...Mat 5:22dzuwa likulowereni muli chikwiyire...Aef 4:26tsono ndidaukwiyira mbadwowo...Aheb 3:10Mulungu adaawakwiyira amene...Aheb 3:17nthawi yoonetsa mkwiyo...Chiv 11:18[onaninso: mkwiyo]

KWIYA (displeased)mwatikwiyira...Mas 60:1pamene Yesu anaona anakwiya...Marko 10:14

KWIYA (furious)munakwiya naye wodzozedwa wanu...Mas 89:38usayanjane ndi munthu wokwiya msanga...Miy 22:24[onaninso: laswa mtima, ukali]

KWIYA (wrath)mudakwiyitsa Chauta...Deut 9:22adawadzudzula ali wokwiya...Mas 2:5choncho ndidakwiya...Mas 95:11amene ndawakwiyira...Yes 10:6ndili wokwiya zedi...Yes 54:8pamene ndinali wokwiya...Yes 60:10ngakhale munali wokwiya...Hab 3:2lisalowe muli chikwiyire...Aef 4:26motero ndili wokwiya...Aheb 3:11munthu wokwiya safikapo...Yak 1:20[onaninso: kuzaza, mkwiyo, udani, ukali]

L

LAKA (overcome)ndalilaka dziko lapansi...Yoh 16:33[onaninso: gonjetsa, pambana]

LAKALAKA (desire)pokhala nacho cholakalaka...Afil 1:23kulakalaka zosayenera...Akol 3:5[onaninso: chikhumbo, chilakolako, funitsitsa, khumba]

LAKWA (offend)ngakhale sindinalakwa...Yob 34:31[onaninso: khumudwitsa, paramula]

LAKWA (offense)ngati ndi kulakwa kwa m’modzi...Aro 5:17a mtima woona ndi osalakwa...Afil 1:10[onaninso: chikhumudwitso,chokhumudwitsa,khumudwa,khumudwitsa, lakwitsa]

LAKWITSA (offense)ndi thanthwe lolakwitsa...Yes 8:14[onaninso: chikhumudwitso,chokhumudwitsa,khumudwa,khumudwitsa, lakwa]

LALIKA (preach)Yesu adayamba kulalika...Mat 4:17koma iwe, kalalike ufumu...Luk 9:60anthu angalalike bwanji...Aro 10:15ife timalalika khristu...1 Akor 9:16zimene timalalika ndizomwezo...1 Akor 15:11

timalalika Yesu Khristu...2 Akor 4:5amene amalalika Khristu...Afil 1:15uzilalika mau a Mulungu...2 Tim 4:2[onaninso: lalikira]

LALIKIDWA (preached)m’dzina lake mau alalikidwe...Luk 24:27m’choonadi Khristu alalikidwa...Afil 1:18kwa ifenso walalikidwa Uthenga...Aheb 4:2[onaninso: lalikira]

LALIKIRA (declare)zakumwamba zimalalikira ulemerero...Mas 19:1ndidzalalikira dzina lanu kwa abale...Mas 22:22kulalikira kuti Yehova...Mas 92:15ndidzalalikira dzina lanu...Aheb 2:12ndipo tidachimva, tikulalikira...1 Yoh 1:3[onaninso: fotokoza, fotokozera]

LALIKIRA (preach)ukaulalikire uthenga...Yon 3:2inu mukazilalikire pa...Mat 10:27wandidzoza kuti ndikalalikire...Luk 4:18[onaninso: lalika]

LALIKIRA (preached)namakalalikira anthu kuti...Marko 6:12adanka nalalika ponseponse...Marko 16:20namalalikira anthu...Mac 8:5Yesuyo tikukulalikirani...Mac 13:38ngakhale ndilalikira kwa ena...1 Akor 9:27akabwera kudzalalikira Yesu...2 Akor 11:4akakulalikirani uthenga wabwino...Agal 1:8nalalikira mizimu inali mndende...1 Pet 3:19[onaninso: lalikidwa]

LALIKIRA (preaches)amene Paulo amamlalika...Mac 19:13kudzalalika Yesu wina...2 Akor 11:4akakulalikirani uthenga wabwino...Agal 1:9tsopano akulalika chikhulupiriro...Agal 1:23

LAMBA (band)atamangira lamba la golidi...Chiv 1:13[onaninso: gulu]

LAMBA (belt)ndi lamba lachikopa mchiuno...Mat 3:4natenga lamba la Paulo...Mac 21:11

LAMBIRA (worship)ndipo mlambireni Iye amene ...Chiv 14:7[onaninso: gwadira, pembedza, pemphera]

LAMULA (command)kuti alamulire ana ake...Gen 18:19Yehova adzakulamulirani...Deut 28:8ndi kusunga malamulo ake...Deut 30:16Yehova adzalamulira chifundo chake...Mas 42:8lamulirani chipulumutso cha Yakobo...Mas 44:4lamulo ili ndinalandira...Yoh 10:18lamulo lake liri moyo...Yoh 12:50muzichita zimene ndikulamulirani...Yoh 15:14mudzachita zimene ndikulamulirani ...2 Ates 3:4[onaninso: mau, uza]

LAMULA (commanded)walamulira m’mawa chiyambire...Yob 38:12analamulira chipangano chake kosatha...Mas 111:9Yehova analamulira dalitsolo...Mas 133:3sanakhoza kulola cholamulidwacho...Aheb 12:20

Page 76: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

LAMULA (reigns)Mulungu amalamula mitundu...Mas 47:8wathu Mphambe akulamulira...Chiv 19:6[onaninso: chita ufumu]

LAMULIRA (grant)lamulirani kuti ana anga awiriwaa...Mat 20:21[onaninso: patsa]

LAMULIRA (rule)mwamuna wakoyo adzakulamulira...Gen 3:16mumalamulira nyanja yayikulu...Mas 89:9adzalamula mwana wa mfulu...Miy 17:2adzalamulira ku Yerusalemu...Mlal 2:19

LAMULO (commandment)malamulo a Yehova ali...Mas 19:8lamulo lanu ndilotakasuka...Mas 119:96malamulo ndi kuunika...Miy 6:23ndi lamulo la anthu analiphunzira...Yes 29:13lamulo lalikuru ndi liti...Mat 22:36ndikupatsani inu lamulo latsopano...Yoh 13:34momwe Atate wandilamulira...Yoh 14:31ndinali wamoyo popanda lamulo...Aro 7:9ukakhale wochimwitsa ndithu mwa lamulo...Aro 7:13ndilo lamulo loyamba lokhala nalo...Aef 6:2sindikulemberani lamulo...1Yoh 2:7ndipo lamulo lake ndi ili...1Yoh 3:23monga tinalandira lamulo...2 Yoh 4ili ndi lamulolo...2 Yoh 6

LAMULO (decree)kunali masiku aja kuti lamulo...Luk 2:1[onaninso: chilamulo, chitsimikizo]

LAMULO (law)pakuchitira mvula lamulo...Yob 28:26pakuti lamulo lidzachokera kwa ine...Yes 51:4amene mumtima mwao muli lamulo...Yes 51:7wolungama ndi ntchito za lamulo...Aro 3:20koma pamene palibe lamulo...Aro 4:15pakuti kufikira nthawi ya lamulo...Aro 5:13popeza simuli a lamulo...Aro 6:14koma mwa lamulo...Aro 7:7lili kulimbana ndi lamulo...Aro 7:23lamulo monga wopanda lamulo...1 Akor 9:21mwa lamulo ndafa ku lamulo...Agal 4:4lamulo siliikika kwa munthu...1 Tim 1:9wakupenyerera m’lamulo langwiro...Yak 1:25chikwanire lamulolo lachifumu...Yak 2:8[onaninso: chilamulo]

LANDA (plunder)motero mudzawalanda zonse...Eks 3:22odutsa amamlanda...Mas 89:41ndi zinthu zolanda...Yes 3:14[onaninso: funkha]

LANDA (plundered)zifuna kulanda moyo...Yer 4:30[onaninso: funkha]

LANDA (plundering)kuti alande chuma chanu...Aheb 10:34[onaninso: kufunkhidwa]

LANDIDWA ZIDA (disarmed)adawalanda zida maufumu...Akol 2:15

LANDIRA (accept)pakuti pemphero lake ndidzalirandira...Yob 42:8alandire zopereka...Mas 20:3

sindidzazilandira...Yer 14:12kodi ine ndidzalandira...Mlal 1:13

LANDIRA (possess)ndi kulandira dziko limene...Yos 1:11[onaninso: gonjetsa, khala]

LANDIRA (obtain)kuti iwonso akalandire chifundo...Aro 11:31koma kuti tilandire chipulumutso...1 Ates 5:9[onaninso: khala, peza]

LANDIRA (obtained)ndipo analandira gawo...Mac 1:17tsopano mwalandira chifundo...Aro 11:30atapirira analandira lonjezolo...Aheb 6:15amene adalandira chikhulupiriro...2 Pet 1:1

LANDIRA (reward)pakuti tilikulandira zoyenera...Luk 23:41[onaninso: bwezera, mphotho]

LANDIRIDWA (acceptable)zolandiridwa ndi Mulungu...1 Pet 2:5[onaninso: komera, kondweretsa, landirika, sankhika]

LANDIRIDWA (accepted)yabwino ndi yolandiridwa...2 Akor 6:2

LANDIRIKA (acceptable)ndicholandirika pamaso pa Mulungu...1 Tim 2:3[onaninso: komera, kondweretsa, landiridwa, sankhika]

LANDITSA (deliver)amlanditse tsopano...Mas 22:8ndidzamlanditsa ndi kumchitira...Mas 91:15nadzatilanditsa m’dzanja lanu...Daniele 3:17adzandilanditsa ku ntchito yonse yoipa...2 Tim 4:18[onaninso: ombola, pulumutsa]

LANDITSA (delivered)pakuti mwalanditsa moyo wanga...Mas 56:13pakuti walanditsa moyo wanga...Yer 20:13amene anatilanditsa...2 Akor 1:10[onaninso: perekedwa, pulumutsa]

LANGA (chasten)uzimlanga mwana wako...Miy 19:18anthu aupanduwa kuti ndiwalange...Hos 10:10amene bambo ake sanamlange...Aheb 12:7ndiwadzudzula ndi kuwalanga...Chiv 3:19pamene ndidadzilanga posala...Mas 69:10ndipo ndalangidwa m’mawa...Mas 73:14Chauta wandilanga koopsa...Mas 118:18ndidalanga ana anu popanda...Yer 2:30azibambo anthu apansi panowa ankatilanga...Aheb 12:10usapepuse kulanga kwake...Yob 5:17ndasenza kulanga kwanu...Yob 34:31muja munalikuwalanga...Yes 26:16ngati Mulungu sakulangani...Aheb 12:8pamene munthu akulandira chilango...Aheb 12:11paja Ambuye amamlanga...Aheb 12:6Ine mwini wake ndidzakulangani...Lev 26:28ndidzawalanga chifukwa cha zolakwa...Hos 7:12chilango chimene chidagwera...Yes 53:5

LANGA (condemn)kulanga kwa amenewo ndikolungama...Aro 3:8[onaninso: tsutsa, weruza]

LANGA (correct)mulanga munthu ndi zomdzudzula...Mas 39:11

Page 77: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

atate a thupi lathu akutilanga...Aheb 12:9ndodo yomlangira...Miy 22:15usamane mwana chilango...Miy 23:13sanamvera kulanga...Yer 2:30[onaninso: langiza]

LANGA (execute)kuti alange mitundu...Mas 149:7mkwiyo wanga ukulangitse...Hos 11:9ndi mphamvu ndithu kukulanga...Aro 13:4[onaninso: chita mlandu]

LANGA (punish)ndidzalanga anthu adziko lapansi...Yes 13:11ndiye ndingapande kulanga...Yer 5:9ndidzalanga onse owazunza...Yer 30:20chilango cha machimo anu...Mali 4:22ndidzawalanga chifukwa cha...Hos 4:9[onaninso: kwapula]

LANGA (punished)mwangotilanga pang’ono...Ezara 9:13ukali wake sukupereka chilango...Yob 35:15kawirikawiri ndinkawalanga...Mac 26:11chilango chao nchakuti...2 Ates 1:9

LANGIZA (admonish)mumatha kulangizana...Aro 15:14[onaninso: chenjeza]

LANGIZA (correct)langiza mwana wako ...Miy 29:17chilangizo cha mchilungamo...2 Tim 3:16[onaninso: langa]

LANGIZA (instruct)wabwino kuti aziwalangiza...Neh 9:20kuyendamo, ndidzakulangiza...Mas 32:8Ambuye, kuti athe kulangiza...1 Akor 2:16

LANGIZA (instructed)iwe walangiza aunyinji...Yob 4:3ndipo ndani analangiza iye...Yes 40:14Mulungu adamlangiza kuti...Aheb 8:5[onaninso: phunzitsidwa]

LANGIZA (instruction)iwe sufuna kulangizidwa...Mas 50:17wanzeru ukamlangiza...Miy 9:9[onaninso: chilangizo, malangizo, mwambo]

LANGIZA (teach)ndidzakulangizani zakumuopa Yehova...Mas 34:11[onaninso: dziwitsa, phunzitsa]

LANKHULA (communed)ndinalankhula ndi mtima...Mlal 1:16

LANULANU (heritage)limenelo kuti likhale lanulanu...Eks 6:8[onaninso: cholowa, gawo]

LASWA MTIMA (furious)analaswa mtima nafuna kuwapha...Mac 5:33[onaninso: kwiya, ukali]

LAWI (flame)lawi la moto lidzaumitsa...Yob 15:30ndi lawi la moto wonyambita...Yes 29:6ngakhale lawi silidzakutentha...Yes 43:2litentha lawi la moto...Yow 2:3ndizunzidwa m’lawi ili lamoto...Luk 16:24omtumikira iye akhale lawi la moto...Aheb 1:7

maso ake ngati lawi lamoto...Chiv 1:14[onaninso: chirangali, lilime, malawi]

LAZARO (Lazarus)wopemphapempha wofotokozedwa mu fanizo...Luk 16:20-25Mlongo wake wa Mariya ndi Marita; woukitsidwa kuchokerakwa akufa...Yoh 11:1-44anakhala nawo pa mgonero...Yoh 12:1,2Ayuda anafuna kumupha...Yoh 12:9-11

LEBANONI (Lebanon)Mbali ya cholowa cha Israeli...Yos 13:5-7sanagonjetsedwe yense...Owe 3:1-3kochokera kwa zida zomangira kachisi ...1 Maf 5:2-18;Ezara3:7ananenedwa mu uneneri...Yes 10:34;29:17;35:2;Ezek 17:3;Hos14:5-7

LEFUKA (faint)anyamata adzalefuka...Yes 40:30adzayenda koma osalefuka...Yes 40:31mtima wanga walefuka...Yer 8:18maso anga alefuka...Mali 2:11

LEFUKA (feeble)manja onse adzalefuka...Ezek 7:17[onaninso: fooka, kutha mphamvu, onda]

LEKA (cease)usana ndi usiku sizidzalekayi...Gen 8:22ndiidulirenji padera ntchito poileka...Neh 6:3apo oipa aleka kumavutika...Yob 3:17lekani kuchita zoipa...Yes 1:16sindileka kuyamika chifukwa cha inu...Aef 1:16sitileka kupembedzera...Akol 1:9ndipo analeka kumanga...Gen 11:8nyanja inaleka kukokoma...Yon 1:15kukumbukira kosalekeza ntchito...1 Ates 1:3tiyamika kosalekeza...1 Ates 2:13pempherani kosaleka...1 Ates 5:17[onaninso: siya]

LEKA (forsake)sindidaleke kutsata malamulo...Mas 119:87osaleka kusonkhana kwathu...Aheb 10:25[onaninso: siya]

LEKANA (divided)sadalekane ali moyo...2 Sam 1:23[onaninso: gawa, gawanika, gawika, gawikana, gawira]

LEKANA (parted)choncho, adalekana nawo...Luk 24:51[onaninso: patukana]

LEMA (weary)iye amene ali wolema...Yes 50:4ndalema ndi kudzikaniza...Yer 6:11ndipo ndalema ndi kupirira...Yer 20:9kuti angandilemetse ndi kudzaidza kwake...Luk 18:5tisaleme pakuchita zabwino...Agal 6:9musaleme pakuchita zabwino...2 Ates 3:13kuti mungaleme ndi kukomoka...Aheb 12:3[onaninso: thodwa, topa]

LEMBA (write)lemba mauwa...Eks 34:27pakuti mundilembera zinthu zowawa...Yob 13:26uwalembe pamtima pako...Miy 7:3lembani munthu uyu wopanda...Yer 22:30

Page 78: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndidzachita kuwalemba m’mitima...Aheb 8:10nzeru zao ndidzawalemba...Aheb 10:16

LEMBA (writing)Mulungu mwini wake anali atalemba...Eks 31:18

LEMBA PA MWALA (engrave)miyala iwiri ya onikisi ndipo ulembepo...Eks 28:9[onaninso: locha]

LEMBEDWA (appointed)popeza masiku ake alembedwa...Yob 14:5[onaninso: ika, yenera]

LEMBEDWA (inscribed)achikhala mauwo adaalembedwa...Yob 19:23ndakulembera iwe pa zikhatho...Yes 49:16

LEMBERA (account)ndidakulembera...Mac 1:1[onaninso: werengera]

LEMEKEZA (bless)ndidzalemekeza Yehova nyengo zonse...Mas 34:1zilemekeze dzina lake loyera...Mas 103:1[onaninso: dalitsa, yamika]

LEMEKEZA (confession)numlekeze Iye, nundiuze tsopano...Yos 7:19[onaninso: chivomerezo]

LEMEKEZA (exalt)ndiye Mulungu wanga ndidzamlemekeza...Eks 15:2[onaninso: kweza, sankha]

LEMEKEZA (glorify)alemekeze Atate wanu wa Kumwamba...Mat 5:16Atate, lemekezani dzina lanu...Yoh 12:28iyeyo adzalemekeza ine...Yoh 16:14Atate Inu, lemekezani Ine ndi Inu nokha...Yoh 17:5imfa imene adzalemekeza nayo Mulungu...Yoh 21:19lemekezani Mulungu mthupi lanu...1 Akor 6:20Khristu sanadzilemekeza yekha...Aheb 5:5koma alemekeze Mulungu m’dzina ili...1 Pet 4:16[onaninso: chitira ulemu, kometsa]

LEMEKEZA (honors)anthu awa andilemekeza...Marko 7:6ndiye wondilemekeza ine...Yoh 8:54

LEMEKEZA (honour)uzilemekeza atate ako...Eks 20:12lemekeza Yehova ndi...Miy 3:9lemekeza atate wako...Mat 15:4onse akalemekeze mwana...Yoh 5:23koma ndilemekeza Atate...Yoh 8:49ngati ine ndidzilemekeza ndekha...Yoh 8:54[onaninso: ulemu]

LEMEKEZEDWA (glorified)pamaso pa anthu onse ndilemekezedwa...Lev 10:3ndipo iwo analemekeza Mulungu wa...Mat 15:31Yesu sanalemekezedwa pa nthawi...Yoh 7:39Yesu analemekezedwa pamenepo...Yoh 12:16mwa ichi alemekezedwa Atate anga...Yoh 15:8Ine ndalemekeza Inu padziko lapansi...Yoh 17:4analemekeza mwana wake Yesu...Mac 3:13m’zonse Mulungu alemekezedwe...1 Pet 4:11

LEMEKEZEKA (honourable)ogulitsa ake ali olemekezeka...Yes 23:8la Yehova, lolemekezeka...Yes 58:13

[onaninso: ulemu]

LEMERA (prosper)monga mzimu wako ulemera...3 Yoh 2[onaninso: dalitsa, lemereza, pindula, phindu]

LEMEREZA (prosper)Yehova anamlemereza m’dzanja...Gen 39:3[onaninso: dalitsa, lemera, pindula, phindu]

LEMETSA (burden)ine sindinalemetsa inu...2 Akor 12:16kuti tingalemetse wina mwa inu...1 Ates 2:9[onaninso: chinthenda, katundu, kukoka, nkhawa]

LEMEZEDWA (enriched)m’zonse munalemezedwa...1 Akor 1:5polemeretsedwa inu m’zonse...2 Akor 9:11

LEMUELI (Lemuel)mfumu yomwe inaphunzitsidwa ndi mai ake...Miy 31:1-31

LENGA (create)ine ndilenga mtendere...Yes 45:7taonani ndilenga kumwamba...Yes 65:17

LENGA (created)Mulungu ndipo adalenga...Gen 1:27muone amene analenga izo...Yes 40:26Woyera wa Israeli wachilenga...Yes 41:20Yehova walenga chatsopano...Yer 31:22sanatilenga kodi Mulungu...Malak 2:10Mulungu wolenga zonse...Aef 3:9zimene Mulungu anazilenga...1 Tim 4:3chifukwa mudalenga zonse...Chiv 4:11[onaninso: lengedwa]

LENGA (formed)panalibe Mulungu wolengedwa...Yes 43:10anthu amene ndinadzilengera...Yes 43:21ndisanakulenge iwe m’mimba...Yer 1:5[onaninso: umba]

LENGA (made)Mulungu adalenga miyuni...Gen 1:16zonsezi mkono wanga wazilenga...Yes 66:2zonse zinalengedwa ndi iye...Yoh 1:3[onaninso: chita, panga]

LENGEDWA (created)potumizira mzimu wanu zilengedwa...Mas 104:30analamulira ndipo zinalengedwa...Mas 148:5mwamuna sanalengedwa...1 Akor 11:9olengedwa mwa Khristu Yesu...Aef 2:10amene analengedwa monga...Aef 4:24mwa Iye mudalengedwa zonse...Akol 1:16[onaninso: lenga]

LEPHERA (fail)kulepheretsa chakumwa...Yes 32:6lilime lao lilephera...Yes 41:17yalephera ntchito ya...Hab 3:17[onaninso: fooka]

LETSA (abstain)akuletsa ukwati...1 Tim 4:3[onaninso: kaniza, lewa, pewa]

LETSA (forbid)Yesu anati, musamuletse ai...Marko 9:39amene angawaletse kubatizidwa...Mac 10:47

Page 79: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

musaletse anthu kulankhula zinthu...1 Akor 14:39popanda wina aliyense womuletsa...Mac 28:31amatiletsa kulalika uthenga...1 Ates 2:16amaletsa anthu ukwati...1 Tim 4:3

LETSA (hindered)anakuletsani ndani kuti musamvere...Agal 5:7[onaninso: letsedwa]

LETSEDWA (hindered)koma ndaletsedwa kufikira lero...Aro 1:13kuti mapemphero anu angaletsedwe...1 Pet 3:7[onaninso: letsa]

LEVI (Levi)mwana wamwamuna wachitatu wa Yakobo ndi Leya...Gen29:34anabwezera kugwiriridwa kwa Dina...Gen 34:25-31uneneri wa Yakobo unamkhudza iye...Gen 49:5-7kholo la Mose ndi Aroni Eks 6:16-27

LEVIYATANI (leviathan)chilombo chija cha leviyatani...Yob 41:1leviyatani amene munamulenga...Mas 104:26

LEWA (abstain)alewe dama...Mac 15:20[onaninso: kaniza, letsa, pewa]

LEYA (Leah)mwana wamkazi wamkulu wa Labani; anapatsidwa kwaYakobo monyenga...Gen 29:16-27sanakondedwa ndi Yakobo koma anabereka ana...Gen29:30-35;30:16-21

LEZA MTIMA (patient)mukhale oleza mtima pa onse...1 Ates 5:14[onaninso: pirira]

LIBINA (Libnah)mzinda wa a Kanani, wolandidwa ndi Yoswa...Yos 10:29,30unapatsidwa kwa zidzukulu za Aaroni...Yos 21:13

LIBIYA (Libya)ananenedwa mu uneneri...Ezek 30:5;Dan 11:43Ayuda ochokera kumeneku analipo pa tsiku la Pentekoste...Mac2:1-10

LIDA (Lydda)kumene Enaya anachiritsidwira...Mac 9:32-35

LIDIA (Lydia)mkazi wa ku Tiatirawotembenuka mtima woyamba wa Paulo wochokera kuUlaya...Mac 16:14,15,40mzinda waku Asiya wamng’ono m’mene munali Efeso,Smirina, Tiatira ndi Sardi...Chiv 1:11

LIKASA LA PANGANO (ark)anapanga likasa...Eks 37:1chokhala palikasa...Lev 16:2tidzitengere likasa la chipangano...1 Sam 4:3ndi likasa la chipangano...Aheb 9:4linaoneka likasa la chipangano...Chiv 11:19[onaninso: chingalawa, chombo]

LIKHIDWA (stricken)pakuti walikhidwa kunja kuno...Yes 53:8[onaninso: kantha, kanthidwa]

LIKWIRA (devour)

kufunafuna wina akamlikwire...1 Pet 5:8icho chikalikwire mwana wake...Chiv 12:4[onaninso: dyana, dyera, idya]

LILIME (flame)monga ngati lilime lamoto...Yes 5:24[onaninso: chirangali, lawi, malawi]

LIMA (plow)wina nkulimapo ndi ng’ombe...Amo 6:12amene wayambapo kulima...Luk 9:62wolima ndiponso wopuntha...1 Akor 9:10

LIMBA MTIMA (bold)koma olungama alimba mtima...Miy 28:1koma m’mene wina alimbika mtimamo...2 Akor 11:21alimbika mtima koposa...Afil 1:14

LIMBA (stand)adzasamira nyumba yake koma yosamlimbira...Yob 8:15koma mkaziyo sadzalimbika kapena...Dan 11:17[onaninso: chirimika, ima, khala, khazikika, tsimikizidwa, uka]

LIMBA (well)olimba safuna sing’anga ayi koma odwala...Mat 9:12[onaninso: bwino, chitsime, koma, komera, ngwiro, pulumutsa]

LIMBANA (against)sitilimbana ndi mwazi...Aef 6:12[onaninso: tsutsana, ukira]

LIMBANA (contend)mulimbanetu chifukwa cha chikhulupiriro...Yuda 3[onaninso: kangana, tsutsana]

LIMBIKA MTIMA (courage)amphamvu limbikani mtima...Deut 31:6anayamika Mulungu nalimbika mtima...Mac 28:15

LIMBIKITSA (edification)zabwino zakumlimbikitsa...Aro 15:2[onaninso: mangirira]

LIMBIKITSA (encouraged)mudzandilimbikitsa ndi chikhulupiriro...Aro 1:12[onaninso: limbikitsidwa]

LIMBIKITSA (exhortation)ngati muli ndi mau olimbikitsa...Mac 13:15ngati nkulimbikitsa ena, tiwalimbikitse...Aro 12:8mau okulimbikitsani mtimawa...Aheb 13:22

LIMBIKITSA (exhorted)ndipo adalimbikitsa abale...Mac 15:32

LIMBIKITSIDWA (encouraged)onse aphunzire ndi kulimbikitsidwa...1 Akor 14:31[onaninso: limbikitsa]

LIMBITSA (confirm)Iye adzakulimbitsani mpaka...1 Akor 1:8[onaninso: tsimikiza]

LIMBITSIRA (establish)limbitsirani mtumiki wanu mau...Mas 119:38[onaninso: khazikitsa]

LIMODZI LA MAGAWO KHUMI (tithes)amalandira limodzilimodzi la magawo khumi m’midzi...Neh

10:37ndi limodzilimodzi la magawo khumi kulonga m’mwemo...Neh12:44

Page 80: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi limodzilomodzi la magawo khumi a tirigu, vinyo...Neh 13:5mubwere nalo limodzilimodzi lonse la magawo khumi, ku...Mal3:10ndipereka limodzi la magawo khumi a zonse ndili nazo...Luk

18:12lamulo lakuti atenge limodzi la magawo khumi kwa

anthu...Aheb7:5anthu ofeka alandira limodzi la magawo khumi kwaAbrahamu...Aheb 7:8Levinso wakulandira limodzilimodzi la magawo khumiadapereka...Aheb 7:9[onaninso: chachikhumi]

LINGA (fortress)thanthwe langa, linga langa...2 Sam 22:2ndi linga langa lolimba...Mas 31:2

LINGALIRA (meditate)anatuluka kulingalira m’munda...Gen 24:63ulingaliremo usana ndi usiku...Yos 1:8ndilingalira mumtima mwanga...Mas 77:6ndidzalingalira pa malangizo...Mas 199:15mlandu musalingalirire chimene...Luk 21:14chitamando china, zilingirire...Afil 4:8

LINGALIRA (meditation)chake amalingalira usana...Mas 104:34chilamulilo chanu, ndilingiriramo...Mas 119:97

LINGALIRA (understood)ndi kulingalira chitsiriziro chao...Mas 73:17[onaninso: mvetsa, phunzira, zindikirika]

LINGANA (compare)sizilingana naye...Miy 3:15zonse tizifunitsa sizilingana naye...Miy 8:11[onaninso: linganiza, linganizidwa]

LINGANA (equal)mwapatsa malipiro olingana...Mat 20:12ankazilinganiza ndi Mulungu... Yoh 5:18sadayese kuti kulingana ndi Mulungu...Afil 2:6

LINGANIZA (compare)kapena kuzilinganiza tokha...2 Akor 10:12timlinganize ndi Yehova...Mas 89:6[onaninso: lingana, linganizidwa]

LINGANIZIDWA (compare)sayenera kulinganizidwa ndi ulemelero...Aro 8:18[onaninso: lingana, linganiza]

LIPENGA (alarm)ndi malipenga oliza...2 Mbir 13:12kudzamveka lipenga...Zefa 1:16

LIRA (cry)nalira, ndikulira kwao kunakwera...Eks 2:23[onaninso: fuula]

LIRA (mourns)ngati munthu wolira maliro...Mas 35:14likulira ndipo likufota...Yes 24:4adzamlira kwabasi...Zek 12:10

LIRA (bemoan)nadzati Nineve wapasuka, adzamlira maliro ndani...Nah 3:7[onaninso: chitira chisoni, lirira, chita maliro]

LIRA MISONZI (grieved)kodi sindinamulirira misonzi...Yob 30:25

[onaninso: mvetsa chisoni, sauka mumzimu]

LIRIRA (bemoan)usankhe kukachita maliro awo kapena kuwalirira...Yer 16:5[onaninso: chitira chisoni, chita maliro, lira]

LISTARA (Lystra)Paulo anakachezakoPaulo anapembedzedwa ndi kugendedwa ndi anthu okhalakumeneko...Mac 14:6-20kwao kwa Timoteo...Mac 16:1,2

LISUNGULU (awl)aboole khutu lake ndi lisungulu...Eks 21:6pamenepo muzitenga lisungulu...Deut 15:17

LITALI (length)m’litali mwake mwa chingalawa...Gen 6:15utali wake ulingana ...Chiv 21:16[onaninso: churuka]

LITSIRO (filth)kuchotsedwa litsiro lam’thupi...1 Pet 3:21[onaninso: zinyatsi, zonyansa]

LOCHA (engrave)ndidzalocha malochedwe ake...Zek 3:9[onaninso: lemba pamwala]

LODZA (bewitched)anakulodzani ndani...Agal 3:1

LOLA (allow)simudzalola wokondedwa...Mas 16:10sangalole kuti...1 Akor 10:13

LOLA (permit)Mzimu wa Yesu sunawalole...Mac 16:7sindidzalola kuti mkazi...1 Tim 2:12ndithu, Ambuye akalola...1 Akor 16:7Mulungu akalola, tidziterodi...Aheb 6:3

LOLA (wills)mukadanena inu, akalola Mulungu...Yak 4:15[onaninso: funa]

LOLOPOKA (delicate)sudzayesedwa wozizira ndi wololopoka...Yes 47:1mkazi wokoma ndi wololopoka...Yer 6:2

LONDOLA (follow)kuti mukalondole mapazi ake...1 Pet 2:21[onaninso: tsata]

LONGOSOKA (behavior)wodziletsa, wolongosoka...1 Tim 3:2[onaninso: khalidwe]

LONJEZA (promise)potsata zimene adawalonjeza...1 Maf 8:56imene Atate anga adalonjeza...Luk 24:49mphatso imene Atate adalonjeza...Mac 1:4adalonjezera inuyo...Mac 2:39achite zimene adalonjeza...Mac 7:17zimene Mulungu adalonjeza...Mac 26:6zimene Mulungu adalonjeza...Aro 4:14odzalandira zimene adalonjeza...Aheb 6:17zimene Mulungu adalonjeza...Aheb 11:39amawalonjeza ufulu...2 Pet 2:19chimene adalonjeza nchimenechi...1 Yoh 2:25[onaninso: lonjezo]

Page 81: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

LONJEZA (promised)monga momwe adalonjezera...Deut 1:11akulandira zimene Mulungu adalonjeza...Aheb 6:12kuti amene adalonjezayo...Aheb 11:11sadalandire zimene Mulungu adawalonjeza...Aheb 11:13zonse zimene Mulungu adalonjeza...2 Akor 1:20amene iye adatilonjeza...2 Pet 1:4

LONJEZO (promise)lonjezolo maziko ake...Aro 4:16Mulungu adapatsa malonjezo...Agal 3:16sapatsidwa chifukwa cha lonjezo...Agal 3:18lonjezo la Mulungu lakuti...Aheb 4:1[onaninso: lonjeza]

LOTA (dream)ndinena naye m’kulota...Num 12:6tinakhala ngati anthu akulota...Mas 126:1akuluakulu anu adzalota...Yow 2:28anaonekera kwa Yosefe m’kulota...Mat 2:13lero m’kulota ine ndasauka...Mat 27:19ndi akulu anu adzalota...Mac 2:17m’kulota kwawo adetsa matupi...Yuda 8

LOTI (Lot)mdzukulu wa Abramu, anayenda naye limodzi...Gen11:27-12:5;13:1analekana ndi Abramu...Gen 13:5-12anapulumutsidwa ndi Abramu...Gen 14:12-16anapulumutsidwa kuchokera ku Sodomu chifukwa cha kukomamtima kwake...Gen 19:1-29ananyengedwa kukuchita chigololo ndi wachibale wake...Gen19:30-38

LOTO (dream)Yosefe ndipo analota loto...Gen 37:5adzauluka ngati loto...Yob 20:8anthu atauka apepula loto...Mas 73:20loto lafika mwakuchuluka ntchito...Mlal 5:3idzafanana ndi loto...Yes 29:7mneneri wokhala ndi loto...Yer 23:28lisakusautse lotoli...Dan 4:19

LOWA (enter)lowani pa zipata zake...Mas 100:4lowani m’matanthwe...Yes 2:10iye alowa mu mtendere...Yes 57:2simudzalowa konse...Mat 5:20lowerani pachipata chophaphatiza...Mat 7:13kuti munthu wolemera akalowe...Mat 19:24lowa iwe mchikondwerero...Mat 25:21kuti mungalowe m’kuyesedwa...Mat 26:41yetsetsani kulowera pakhomo...Luk 13:24wosalowa m’khola la nkhosa...Yoh 10:1ngati adzalowa mpumulo...Aheb 4:3chakulowa m’malo opatulika...Aheb 10:19munthu amakhoza kulowa...Chiv 15:8ndiponso kulowa mumzinda...Chiv 22:14

LOWA (entered)satana adamulowa Yudasi...Luk 22:3uchimo udalowa m’dziko lapansi...Aro 5:12nisizinalowa mumtima mwa munthu...1 Akor 2:9adatitsogolera kale nkulowamo...Aheb 6:20nkukalowa kamodzi kokhako...Aheb 9:12munthu akalowera pa Ine...Yoh 10:9nkukalowa mpaka kumalo opatulika...Aheb 6:19

LUKA (Luke)“sing’anga wokondedwa”...Akol 4:14mnzake wa Paulo wotsiriza...2 Tim 4:11

LUMA (bit)

ndipo zinaluma anthu...Num 21:6[onaninso: cham’kamwa]

LUMA (bite)njoka ikaluma...Mlal 10:11koma ngati mulumana...Agal 5:15

LUMBIRA (oath)ndidalonjeza makolo anu molumbira...Yer 11:5adakananso molumbira kuti...Mat 26:72Abrahamu, kholo lathu molumbira...Luk 1:73ndipo adapangana molumbira...Mac 23:12[onaninso: lumbiro, themberero]

LUMBIRA (oaths)kuti usalumbire monama...Mat 5:33koma chifukwa cha malumbiro...Mat 14:9

LUMBIRO (oath)chifukwa cha lumbiro...Mlal 8:2[onaninso: lumbira]

LUMIKIZA (composed)Mulungu analumikizitsa thupi...1 Akor 12:24

LUNGAMA (truth)zake zonse ndi zolungama...Deut 32:4amene amachita zolungama...Mas 15:2kulungama kwanu...Mas 119:142kuweruza kolungama...Yes 59:14[onaninso: choona, choonadi, zoona]

LUNJIKA (equity)Inu mukhazikitsa zolunjika...Mas 99:4chiweruzo ndi zolunjika...Miy 1:3[onaninso: fana, ongoka, onongeka]

LUNTHA (understanding)uphungu ndi luntha ali nazo...Yob 12:13ndi luntha malo ake ali kuti...Yob 28:12kupatukana nacho choipa ndiko luntha...Yob 28:28ndipo sanaigawira luntha...Yob 39:17osachirikizika pa luntha lako...Miy 3:5naika zamwamba ndi luntha...Miy 3:19kudziwa Woyerayo ndiko luntha...Miy 9:10wosunga luntha adzapeza zabwino...Miy 19:8nzeru ndi mwambo ndi luntha...Miy 23:23[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kumvera, kuzindikira,

luso, Foursquare Missions PressFoursquare Missions PressFoursquareMissions PressFoursquare Missions PressFoursquare MissionsPressFoursquare Missions Pressmvetsa, nzeru]

LUPIYA LATHEKA (denarius)pa lupiya latheka...Mat 20:2anadza nalo kwa iye lupiya latheka...Mat 22:19muyeso watirigu wogula ndi lupiya...Chiv 6:6

LUSO (understanding)ndi luso anayala thambo...Yer 51:15[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kumvera, kuzindikira,luntha, mvetsa, nzeru]

M

MAAKA (Maacah)ufumu waung’ono wa Siria pafupi ndi phiri la Heremoni...Deut3:14sanatengedwe ndi Israeli...Yos 13:13— mkazi wa Davide; mai ake a Abisalomu...2 Sam 3:3— mkazi wa Rehoboamu, mai ake a mfumu Abiya...2 Mbir11:18-21anapanga fano; anapatsidwa udindo wa ufumukazi...1 Maf

Page 82: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

15:13

MAAPULOSI (apples)munditsitsimutse ndi maapulosi...Nyi 2:5[onaninso: zipatso zagolidi]

MABERE (breasts)madalitso a mabere...Gen 49:25inu pa bere la mai wanga...Mas 22:9ndi mabere a zitonthozo...Yes 1:6ndi mabere amene munayamwa...Luk 11:27[onaninso: mawere]

MABUKU (books)pakuti saleka kulemba mabuku...Mlal 12:12malo a mabuku...Yoh 21:25anasonkhanitsa mabuku...Mac 19:19mabuku anatsegulidwa...Chiv 20:12

MABWALO (courts)akhale m’mabwalo anu...Mas 64:4ndi kufuna mabwalo a Yehova...Mas 84:2adzaphuka m’mabwalo a Mulungu...Mas 92:13ndi kumabwalo ake ndi chilemekezo...Mas 100:4m’mabwalo a kachisi wanga...Yes 62:9

MABWERERO (backslidings)mabwerero ako adzakudzudzula...Yer 2:19ndidzachiritsa mabwerero anu...Yer 3:22ndi mabwerero ao achuluka...Yer 5:6pakuti zobwerera zathu zachuluka...Yer 14:7

MACHITIDWE (acts)analangiza Mose machitidwe...Mas 103:7

MACHITIDWE (deeds)mulalikire machitidwe ake...Yes 12:4[onaninso: ntchito]

MACHITIDWE (ways)chiyambi cha machitidwe a Mulungu...Yob 40:19[onaninso: njira]

MACHIMO (sins)machimo anga ndangati...Yob 13:23mwaika machimo athu...Mas 90:8machimo anu adakulekanitsani...Yes 59:2kusiya machimo ndi zolakwa...Dan 9:24ndikadzawachotsera machimo...Aro 11:27adafera machimo athu...1 Akor 15:3ndipo mukadali m’machimo...1 Akor 15:17adatikhululukira machimo...Aef 1:7amene machimo ao...1 Tim 5:24ndi kuchotsa machimo...Aheb 9:28adzatikhululukira machimo...1 Yoh 1:9nsembe yopepesera machimo...1 Yoh 2:2wakukhululukirani machimo...1 Yoh 2:12

MADALITSO (blessings)madalitso ali pamutu pa...Miy 10:6madalitso a Yehova...Miy 10:22[onaninso: dalitso]

MADANDAULO (complaining)chitani zonse kopanda madandaulo...Afil 2:14

MADYERERO (banquet)ku madyerero ndidawakonzera...Este 5:4kulowa mnyumba ya madyerero...Dan 5:10[onaninso: phwando]

MADYERERO (feast)

muchitire Yehova madyerero...Num 29:12kupita ku nyumba ya madyerero...Mlal 7:2[onaninso: chikondwerero, phwando]

MADZI AKULU (flood)muwatenga ngati ndi madzi akulu...Mas 90:5[onaninso: chigumula]

MADZI (water)chigumula cha madzi...Gen 49:4pokupatsani madzi ndi chakudya...Eks 23:25chakudya pang’ono ndi madzi...1 Maf 22:27monga madzi amaphwa...Yob 14:11monganso madzi amayenda...Yob 14:19wakumwa chosalungama ngati madzi...Yob 15:16otopa sudawapatse madzi...Yob 22:7amasunga madzi ambiri...Yob 26:8watayika ngati madzi...Mas 22:14loguga ndi lopanda madzi...Mas 63:1magazi ao ngati madzi...Mas 79:3imwa madzi a m’chitsime...Miy 5:15madzi akuba ndiwo...Miy 9:17adzachotsa madzi onse...Yes 3:1akufunafuna madzi...Yes 41:17ndidzathira madzi pa...Yes 44:3natipatsa ife madzi a ndulu...Yer 8:14diso langatu likudza madzi...Mali 1:16adzaweyeseka ngati madzi...Ezek 7:17sunandipatsa madzi...Luk 7:44chifukwa panali madzi ambiri...Yoh 3:23akadakupatsa madzi amoyo...Yoh 4:10mitsinje ya madzi amoyo...Yoh 7:38panaturuka pomwepo mwazi ndi madzi...Yoh 19:34pali munthu akhoza kuletsa madzi...Mac 10:47kumsambitsa madzi ndi mau...Aef 5:26motero madzi amchere sakhoza...Yak 3:12anapulumutsidwa mwa madzi...1 Pet 3:20Mzimu ndi madzi, ndi mwazi...1 Yoh 5:8mitambo yopanda madzi...Yuda 12atenge madzi amoyo kwaulere...Chiv 22:17

MADZI (waters)napanda madzi ali m’nyanjamo...Eks 7:20taona atsekera madzi...Yob 12:15anditsogolera ku madzi odikha...Mas 23:2chinkana madzi ake akokoma...Mas 46:3madzi afikira moyo wanga...Mas 69:1akadatimiza madziwo...Mas 124:4wothirira madzi nayenso...Miy 11:25ndani wamanga madzi...Miy 30:4ponya zakudya zako pamadzi...Mlal 11:1chitsime cha madzi amoyo...Nyi 4:15madzi ambiri sangazimitse...Nyi 8:7monga madzi adzadza...Yes 11:9ndipo madzi adzaphwa...Yes 19:5chifukwa ndipatsa madzi m’chipululu...Yes 43:20ndinalumbira kuti madzi a Nowa...Yes 54:9idzani kumadzi ndi opanda...Yes 55:1zitsime zosakhalamo madzi...Yer 2:13madzi anayenda pamwamba...Mali 3:54mkokomo wa madzi ambiri...Ezek 43:2kuti madzi amoyo adzaturuka...Zek 14:8ku akasupe a madzi amoyo...Chiv 7:17magawo atatu a madzi...Chiv 8:11

MAERE (lot)aligawe ndi kuchita maere...Num 26:55udzachita nafe maere...Miy 1:14maere aponyedwa pa mfunga...Miy 16:33

MAFANIZO (parables)enawa amazimvera m’mafanizo...Luk 8:10

Page 83: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: fanizo]

MAFANO (idols)choperekedwa kwa mafano...1 Akor 8:7anthu ndi mafano chabe...Mas 96:5mafano ao ndi a siliva...Mas 115:4dziko lao ladzala ndi mafano...Yes 2:8kuyaluka nao mafano...Yer 50:38akupembedza fano lake...Ezek 8:12mafano a m’nyumba...Zek 10:2zidaperekedwa kwa mafano...Mac 15:20umanyansidwa ndi mafano...Aro 2:22idaperekedwa kwa mafano...1 Akor 10:28osapembedza mafano...1Yoh 5:21ndi mafano a golide...Chiv 9:20

MAFUNDE (billows)mafunde anu ang’onoang’ono ndi akuruakuru...Mas 42:7mafunde anu onse anyondonyondo andimiza...Yon 2:3

MAFUPA (bones)mudzakwera nawo mafupa...Gen 50:25nanthunthumira nako mafupa...Yob 4:14mafupa ake akunga...Yob 40:18ndikhoza kuwerenga mafupa...Mas 22:17ndi mafupa anga apuwala...Mas 31:10mafupa anga anakalamba...Mas 32:3ngakhale makulidwe a mafupa...Nyi 11:5mafupa ouma inu...Ezek 37:4mafupa awa ndiyo nyimbo yonse ya...Ezek 37:11ndi mafupa a anthu akufa...Mat 23:27nalamulira za mafupa ake...Aheb 11:22

MAFUTA AMKAKA (butter)anatenga mafuta amkaka...Gen 18:8mposalala ngati mafuta amkaka...Mas 55:21potakasa mkaka, mafuta ayengekako...Miy 30:33anamtengera mafuta a mkaka...Ower 5:25padakhathamira ndi mafuta a mkaka...Yob 29:6

MAFUTA A M’MAFUPA (marrow)mfundo ndi mafuta a m’mafupa...Aheb 4:12

MAFUTA (oil)za mafuta odzodzera...Eks 25:6sindingasiye mafuta angawa...Ower 9:9mafuta pang’ono msupa...1 Maf 17:12padakhatamira ndi mafuta amkaka...Yob 29:6mwadzodza ndi mafuta...Mas 92:10mafuta odzola kuti...Mas 104:15ngati mafuta a mtengo wapatali...Mas 133:2ndidzakuyesa mafuta a pamutu...Mas 141:5kapena mitsinje ya mafuta...Mik 6:7nsupa yagalasi ya mafuta...Mat 26:7pakuti mafuta awa akadagulitsa...Mat 26:9ndi kumdzodza ndi mafuta...Yak 5:14usaononge mitengo ya mafuta...Chiv 6:6

MAFUTA (perfume)mafuta ndi zonunkhira...Miy 27:9likundikumbutsa za mafuta...Nyi 1:8

MAGALETA (chariots)adapinda mikombero ya magaleta...Eks 14:25ena amatamira magaleta...Mas 20:7magaleta amphamvu zikwi...Mas 68:17

MAGANIZO (thoughts)munthu wosalungama asiye maganizo ake...Yes 55:7pakuti maganizo anga sali maganizo anu...Yes 55:8maganizo ako achabe agona mwako...Yer 4:14pakuti mumtima muchokera maganizo oipa...Mat 15:19

anakhala opanda pake m’maganizo ao...Aro 1:21[onaninso: malingaliro, zolingalira, zolingirira]

MAGOGI (Magog)anthu m’gulu la zizukulu za Yafeti...Gen 10:2ogwirizana ndi Gogi...Ezek 38:2oimirira adani otsiriza...Chiv 20:8

MAGUWA ANSEMBE (altars)misanja yake ndi maguwa ansembe ake...2 Maf 18:22pa maguwa ansembe...Mas 84:3za maguwa ansembe...Yer 17:1ndi maguwa anu ansembe adzakhala...Ezek 6:4anachulukitsa maguwa ansembe...Hos 8:11inde maguwa awo ansembe akunga...Hos 12:11ndidzalanganso maguwa ansembe...Amo 3:14nagwetsa maguwa ansembe...Aro 11:3

MAHANAIMU (Mahanaim)dzina lopatsidwa ndi Yakobo la malo opatulika...Gen 32:2unasanduka mzinda waukulu wa Isiboseti...2 Sam 2:8-29Davide anathawirako pa thawi ya kuukira kwa Abisalomu 2Sam 17:24,27

MAHEMA (canopies)mdimawo ngati mahema...2 Sam 22:12

MAHEMA (tents)okhala m’mahema akuweta...Gen 4:20mahema ako ngokoma...Num 24:5mahema a achifwamba...Yob 12:6koposa kugonera m’mahema a choipa...Mas 84:10ndigonera m’mahema a Kedara...Mas 120:5adzayamba kupulumutsa mahema a Yuda...Zek 12:7

MAI (mother)chifukwa anali amai a...Gen 3:20namsandutsa mai wosangalala...Mas 113:9m’modzi yekha mwa amai ake...Nyi 6:9kuti mai anga asanduke manda...Yer 20:17atate ake ndi amai ake...Mat 19:5nawa amai ako...Yoh 19:27mfulu, ndipo ndiye mai...Agal 4:26amai wa achigololo...Chiv 17:5

MAI (woman)ukumuwona maiyu...Luk 7:44mai wachisamariya uja...Yoh 4:9adabwera ndi mai...Yoh 8:3adaona amai ake...Yoh 19:26mai atavala dzuwa...Chiv 12:1lidamthandiza maiyo...Chiv 12:16[onaninso: mkazi]

MAITANIDWE (calling)penyani maitanidwe anu...1 Akor 1:26yense akhale m’maitanidwe...1 Akor 7:20muyende koyenera maitanidwe...Aef 4:1chiyembekezo chimodzi cha maitanidwe...Aef 4:4natiitana ife ndi maitanidwe oyera...2 Tim 1:9olandirana nawo maitanidwe...Aheb 3:1[onaninso: kuitana]

MAIWE (pools)chikhale ndi maiwe a madzi...Mas 107:6maiwe a ku Hesiboni...Nyi 7:4

MAKALA (coals)adzawagwetsera makala...Mas 11:6makala a moto anali lawilawi...Mas 18:8makala a moto awagwere...Mas 140:10munthu angathe kuponda makala a moto...Miy 6:28

Page 84: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

adzaunjike makala a moto...Miy 25:22pakutero udzaunjika makala...Aro 12:20

MAKALATA (epistles)tikhale ndi makalata ochitira...2 Akor 3:1chimodzimodzi m’makalata ake onse...2 Pet 3:16

MAKANDA (babes)m’kamwa mwa makanda...Mas 8:2ndipo ana amakanda ndiwo adzawalamulira...Yes 3:4ndipo munaziululira zomwe kwa makanda...Mat 11:25mkamwa mwa makanda ndi oyamwa...Mat 21:16koma monga athupi, monga makanda mwa Khristu...1 Akor 3:1monga makanda atsopano...1 Pet 2:2

MAKHALIDWE (character)makhalidwe ovomerezeka amabweretsa...Aro 5:4tilibe makhalidwe otere...1 Akor 11:16m’mene anthu ayenera kukhalira...1 Tim 3:15aonetse ndi makhalidwe ake abwino...Yak 3:13kusiyana nawo makhalidwe anu achabe...1 Pet 1:18azikopeka ndi makhalidwe a...1 Pet 3:1

MAKHALIDWE (custom)tiribe makhalidwe otere... 1 Akor 11:16[onaninso: mwambo]

MAKIPERA (Machpelah)munda wokhala ndi phanga, wogulidwa ndi Abrahamu...Gen23:9-18pamene Sara ndi Abrahamu anaikidwa...Gen 23:19;25:9,10Isake, Rabeka, Leya ndi Yakobo anaikidwanso pamenepa...Gen49:29-31

MAKIRI (Machir)mwana yekhayo wa Manase...Gen 50:23woyambitsa banja la Amakiri...Num 26:29anagonjetsa Giliyadi...Num 32:39,40

MAKOLO (fathers)Mulungu wa makolo athu...Ezara 7:27makolo athu ankadalira inu...Mas 22:4makolo athu adatiuza...Mas 44:1tachimwa monga makolo athu...Mas. 146:9makolo athu ankadya mana...Yoh 6:31ndi zidzukulu za makolo athu...Aro 9:5makolo athu onse anali...1 Akor 10:1[onaninso: atate]

MAKOLO (forefathers)makolo ao amene adakana...Yer 11:10nkuyamba kuzunza makolo athu...Mac 7:19momwe ankachitira makolo anga...1 Tim 1:3

MAKOLO (parents)ana adzaukira makolo ao...Mat 10:21kapena abale kapena makolo...Luk 18:29zoipa, samvera makolo...Aro 1:30ana kusungira makolo ao...2 Akor 12:14

MAKOMA (walls)makoma a mzindawo...Yos 6:5[onaninso: malinga]

MAKOMBO (fragments)anatola makombo otsala...Mat 14:20nakhuta onsewo, natola makombo...Luk 9:17mitanga khumi ndi iwiri ndi makombo...Yoh 6:13

MAKOMO (doors)ndiponso pamakomo polowera...Miy 8:3[onaninso: zitseko]

MAKOSI (necks)atakweza makosi ao...Yes 3:16[onaninso: khosi]

MAKUTU (ears)wotseka makutu ake polira...Miy 21:13lemeretsa makutu ao...Yes 6:10amene ali ndi makutu akumva amve...Mat 11:15m’makutu ao munali mogontha...Mat 13:15makutu ake akumva pembedzero...1 Pet 3:12[onaninso: khutu]

MAKWANIRIDWE (fullness)a makwaniridwe a nyengozo...Aef 1:10[onaninso: chidzalo, khuta, kudzala, kudzaza, kwaniridwa]

MAKWERERO (degrees)m’tsogolo makwerero khumi...2 Maf 20:9

MALAKI (Malachi)Mneneri ndi wolemba buku...Mal 1:1

MALAMULO (commandments)malamulo a Yehova ali oyera...Mas 19:8malamulo ndi kuunika...Miy 6:23ngati tisamalira kuchita malamulo...Deut 6:25kwa iwo akukumbukira malamulo ake...Mas 103:18musandibisire malamulo anu...Mas 119:19chifukwa chake ndikonda malamulo anu...Mas 119:127pa malamulo awa awiri...Mat 22:40iye wakukhala nawo malamulo anga...Yoh 14:21munthu amene asunga malamulo ake...1 Yoh 3:24malamulo a Yehova ali angwiro...Mas 19:7malamulo a Mulungu wake...Mas 37:31

MALANGIZO (correction)ndi chilangizo cha Ambuye...Aef 6:4wosamala malangizo amayenda...Miy 10:17[onaninso: malango]

MALANGIZO (instruction)nzeru ndi malangizo...Miy 1:7muzimva malangizo kuti...Miy 8:33kumvera malangizo...Miy 19:27ukhale pa malangizo...Miy 23:12[onaninso: chilangizo, langiza, mwambo]

MALANGO (correction)usanyoze malango a Chauta...Miy 3:11[onaninso: malangizo]

MALAWI (flame)adamuonekera ngati malawi...Eks 3:2umapsera m’malawi a moto...Yes 5:24ndi malawi a moto woononga...Yes 29:6malawi ake sadzakutentha...Yes 43:2kumbuyo kwake malawi a moto...Yow 2:3[onaninso: chirangali, lawi, lilime]

MALAWI (flames)ligawa malawi a moto...Mas 29:7

MALAYA (garment)malaya abwino a ku Babulo...Yos 7:21monga wovula malaya...Miy 25:20idzasuka monga malaya...Aheb 1:11malaya ochitidwa mawanga...Yud 23

MALEKEZERO (ends)malekezero onse a dziko...Mas 22:27kufikira malekezero a dziko...Mac 13:47mpaka kumalekezero a dziko...Aro 10:18

Page 85: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: mathero, matsiriziro]

MALEMBO (scriptures)adaneneratu malembo...Luk 4:21mau a m’malembo ngoona...Yoh 10:35malembo akuti bwanji...Aro 4:3malembo akunenetsa…Agal 3:22olembedwa m’malembo...2 Pet 1:20simudziwa malembo…Mat 22:29zomwe malembo adanena...Marko 14:49wodziwa malembo kwambiri...Mac 18:24wawazolowera malembo...2 Tim 3:15

MALICHERO (basket)malichero atatu a mikate...Gen 40:16malichero asanu ndi awiri...Mat 15:37[onaninso: mitanga]

MALIKISUWA (Malchishua)mwana wamwamuna wa Saulo...1 Sam 14:49anaphedwa ku Gilibowa...1 Sam 31:2

MALINGA (bulwarks)penyetsetsani malinga ake...Mas 48:13chikhale machemba ndi malinga...Yes 26:1

MALINGA (walls)nkuusiya wopanda malinga...Miy 25:28ndi zipupa ndi malinga...Yes 26:1malinga a mzinda wa...Aheb 11:30[onaninso: makoma]

MALINGALIRO (thoughts)malingaliro ake onse akuti palibe Mulungu...Mas 10:4[onaninso: maganizo, zolingalira, zolingirira]

MALIPIRO (wages)ine ndidzakulipirani...Eks 2:9ndiye malipiro a anthu...Miy 10:16ogwira ntchito yolipira...Yes 19:10malipiro a anthu...Hag 1:6antchito aja uwalipire...Mat 20:8muzikhutira ndi malipiro anu...Luk 3:14ngwoyenera kulandira malipiro...Luk 10:7analandira malipiro...Aro 4:4malipiro amene uchimo...Aro 6:23ngwoyenera kulandira malipiro...1 Tim 5:18ndalama za malipiro...Yak 5:4

MALIRE (boundary)ndikukulitsa malire ako...Eks 34:24munaika malire kuti...Mas 104:9akhalitsa malire anu...Mas 147:14

MALIRO (burial)ndiponso alibe maliro...Mlal 6:3[onaninso: ika m’manda]

MALISECHE (naked)onse anali maliseche...Gen 2:25adazindikira kuti alimaliseche...Gen 3:7ndidatulukamo maliseche...Yob 1:21wakhala akuyenda maliseche...Yes 20:3ndidaali wamaliseche, inu...Mat 25:36nkukhala ali maliseche...Marko 14:52tisadzapezeke maliseche...2 Akor 5:3akhungu ndi amaliseche...Chiv 3:17

MALISECHE (nakedness)anauona umaliseche wa atate...Gen 9:22mchisanu ndi umaliseche...2 Akor 11:27muvale ndi kubisa maliseche...Chiv 3:18

[onaninso: usiwa]

MALIZA (end)udzakhalira komaliza...Yob 8:7ndithu chimalizo chinali...Mali 4:18chilango chako chomaliza...Ezek 21:25[onaninso: chimaliziro, chitsiriziro, itha, mathero, matsiriziro,tsiriza]

MALIZA (finish)mudzi wako wopatulika, kumaliza...Dan 9:24ngati alinazo zakuimaliza...Luk 14:28[onaninso: tsiriza]

MALO OTSETSEREKA (cliff)mobisika motsetsereka...Nyi 2:14

MALO A ANTHU AKUFA (hades)adzakutsitsa mpaka kumalo a anthu akufa...Mat 11:23makomo a dziko la akufa...Mat 16:18ankazunzika kumalo a anthu akufa...Luk 16:23simudzandisiya kumalo a anthu akufa...Mac 2:27malo a anthu akufa makiyi ake ali...Chiv 1:18imfa ija ndi malo a anthu akufa...Chiv 20:14

MALO OKHALA (abode)adasiya malo amene Mulungu...Yuda 6

MALO (ground)pakuti pamalo pameme upondapo...Eks 3:5[onaninso: munda, nthaka]

MALO (place)malo waimapowo ngoyera...Eks 3:5osamdziwanso malo...Yob 7:10onse opita ku malo...Mlal 3:20kubwerera kumka ku malo...Hos 5:15muno mudzaone malo...Mat 28:6mau anga alibe malo...Yoh 8:37alimo malo okhalamo...Yoh 14:2kuti apite ku malo...Mac 1:25

MALO (room)anasowa malo m’nyumba...Luk 2:7ndipo malo atsalapo...Luk 14:22[onaninso: chipinda]

MALONDA (business)wina kumalonda ake...Mat 22:5[onaninso: ntchito]

MALONDA (merchandise)amazindikira kuti malonda...Miy 31:18nyumba yochitiramo malonda...Yoh 2:16

MALONI (Mahlon)mwamuna wa Rute; wopanda mwana, Rute 1:2-5

MALOTO (dreams)maloto akachuluka...Mlal 5:7analota maloto ndi mzimu wake...Dan 2:1

MALUWA (flowers)maluwa aoneka pansi...Nyi 2:12

MAME (dew)Mulungu akupatse iwe mame...Gen 27:28m’mene mame amangogwa...Deut 33:28kuli ngati mame pa udzu...Miy 19:12mame ako akunga mame a pamasamba...Yes 26:19ngati mame okamuka msanga...Hos 6:4ngati mame ochoka kwa Chauta...Mik 5:7

Page 86: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MAMULE (Mamre)mzinda kapena boma pafupi ndi Hebroni...Gen 23:19Abramu anakhala pa mitengo yake ya thundu...Gen 13:18

MANA (manna)ana a Israeli anadya mana...Eks 16:35ndipo anawavumbitsira mana...Mas 78:24atate athu anadya mana...Yoh 6:31ndidzampatsa mana obisika...Chiv 2:17

MANASE (Manasseh)mwana woyamba wamwamuna wa Yosefe...Gen 41:50,51anatengedwa ndi Yakobo...Gen 48:5,6anataya ukulu wake kwa Efremu...Gen 48:13-20— Fuko:linawerengedwa...Num 1:34,35theka la fuko lake linakakhala kum’mawa kwa Yordane...Num32:33-42fuko lake linathandiza Yoswa kugonjetsa Akanani...Yos1:12-18malo anapatsidwa kwa theka la fuko lake lokhalakummwera...Yos 17:1-13theka la fuko la kummawa linamanga guwa la nsembe...Yos22:9-34ena a iwo anathandiza Davide...1 Mbir 12:19-31— Mfumu yoipa ya Yuda; mwana wa Hezekiya...2 Maf21:1-18;2 Mbi 33:1-9anagonjetsedwa ndi kutengeredwa ku Babulo; analapa ndipoanabwezeretsedwa2 Mbi 33:10-13anachotsa mafano ndi maguwa a nsembe...2 Mbir 33:14-20

MANDA (grave)munthu wolowa kumanda sabwerako...Yob 7:9ndicho kukakhala ku manda...Yob 17:13kuti ndingatsikire kumanda...Mas 30:3moyo wanga ku ulamuliro wa ku manda...Mas 49:15kumanda kumene ukupitako kulibe...Mlal 9:10adamkonzera manda ake pakati...Yes 53:9kodi iwe manda, kuononga kwako...Hos 13:14kunalibe malo a manda...Eks 14:11manda adatsekuka...Mat 27:52chifukwa muli ngati manda...Luk 11:44amene ali m’manda adzamva mau...Yoh 5:28

MANDA (pit)inde wasendera kufupi kumanda...Yob 33:22ndidzafanana nao iwo akutsikira kumanda...Mas 28:1muja ndinamgwetsera kumanda...Ezek 31:16[onaninso: chionongeko, dzenje, phompho]

MANGA PAKAMWA (muzzle)musaimange pakamwa...Deut 25:4usaimange pakamwa...1 Tim 5:18

MANGA MCHUUNO (gird)dzimangireni lupanga lanu mchuuno...Mas 45:3Mulungu, ndidzakumanga mchuuno...Yes 45:5mnyamata umadzimangira wekha mchuuno...Yoh 21:18mwa ichi, podzimanga mchiuno...1 Pet 1:13chopukutira, nadzimanga mchuuno...Yoh 13:4atamangira lamba la golide...Chiv 1:13

MANGA (bind)kodi ungamange gulu la nsangwe...Yob 38:31kodi ukhoza kumanga njati...Yob 39:10uzimange pakhosi pako...Miy 3:3uwamange pa zala zako...Miy 7:3manga umboni...Yes 8:16wakantha, nadzitimanga...Hos 6:1chimene ukamanga padziko lapansi...Mat 16:19

mumange iye manja ndi miyendo...Mat 22:13inde amanga akatundu olemera...Mat 23:4

MANGA (bond)ndikukulowetsa mchimango...Ezek 20:37kwa chimangiriro cha mtendere...Aef 4:3ndicho chomangirira cha mtima...Akol 3:14

MANGA (build)tiyeni timange mudzi...Gen 11:4udzandimangira nyumba yoti ndikhalemo...2 Sam7:5kumangira dzina la Yehova Mulungu wa Israeli...1 Maf 8:17Yehova adzakumangira banja...1 Mbir 17:10Solomo mwana wako ndiye adzandimangira...1 Mbir 28:6alinayo mphamvu ya kumanga...2 Mbir 2:6akapanda kumanga nyumba...Mas 127:1ndi mphindi ya kumanga...Mlal 3:3mudzandimangira nyumba...Yes 66:1ndipo ndidzamangitsa mudzi...Yer 24:6amanga Ziyoni ndi mwazi...Mik 3:10ndi kumanganso mabwinja...Malak 1:4munthu uyu anayamba kumanga...Luk 14:30mudzandimangira nyumba yotani...Mac 20:32chiri ndi mphamvu yakumanga...Mac 20:32kuti ndisamange nyumba...Aro 15:20ndazigumula ndizimanganso...Agal 2:18

MANGA (built)nzeru idamanga nyumba...Miy 9:1ndidaamanga nyumba …Mlal 2:4ndidaumanga kuti...Dan 4:30wanzeru amene adamanga...Mat 7:24munthu wopusa amene adamanga...Mat 7:26zimene munthu adamanga...1Akor 3:14ndinu womangidwa pamodzi...Aef 2:20mupitirire kumanga moyo...Akol 2:7nyumba iliyonse imangidwa...Aheb 3:4yoti Mulungu amangire nyumba...1 Pet 2:5

MANGIDWA (armed)inu munandimanga...2 Sam 22:40

MANGIRIRA (building)podzimangirira nokha pa chikhulupiriro...Yuda 20[onaninso: nyumba]

MANGIDWA (bound)ngakhale kumangidwa...Yes 1:6chikhala chomangidwa kumwamba...Mat 16:19womwalirayo anatuluka womangidwa...Yoh 11:44ku Yerusalemu womangidwa...Mac 20:22cha Israeli ndamangidwa...Mac 28:20mkazi wokwatidwa amangidwa...Aro 7:2kodi wamangidwa kwa mkazi...1 Akor 7:27nammanga iye zaka chikwi...Chiv 20:2koma mau a Mulungu samangika...2 Tim 2:9

MANGIRIRA (edification)alankhula ndi anthu chomangirira...1 Akor 14:3muchite zonse kukumangirira...1 Akor 14:26anatipatsa Ambuye kukumangirira...2 Akor 10:8anandipatsa ine wakumangirira...2 Akor 13:10[onaninso: limbikitsa]

MANGIRIRA (edifies)lilime, adzimangirira yekha...1 Akor 14:4koma sizimanga zonse...1 Akor 10:23ndipo mangiriranani...1 Ates 5:11chikondi chimangirira...1 Akor 8:1

MANJA (arms)ndi pansipo pali manja osatha...Deu 33:27

Page 87: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

zipsera izi m’manja mwako...Zek 13:6ndi kuika manja ake pa ito...Marko 10:16anamlandira iye m’manja mwake...Luk 2:28

MANJA (hand)mundilanditse m’manja a adani...Mas 18:35[onaninso: dzanja, mkono, pafupi, yandikira]

MANJA (hands)koma manja ndi manja...Gen 27:22ndi manja ake omwe apolesa...Yob 5:18ndi kuyeretsa manja anga...Yob 9:30manja anu anandiumba...Yob 10:8ndiboola m’manja anga ndi...Mas 22:16ndipo manja ake anaumba dziko...Mas 95:5ntchito yako, iye alibe manja...Yes 45:9uli ndi manja awiri kapena mapazi...Mat 18:8penyani manja anga ndi mapazi...Luk 24:39anga okha komanso manja...Yoh 13:9manja anga awa adatumikira...Mac 20:34nagwire ntchito yokoma ndi manja...Aef 4:28ndi kukweza manja oyera...1 Tim 4:14pamodzi ndi kuika kwa manja...1 Tim 4:14kugwa m’manja a Mulungu...Aheb 10:31

MANKHUSU (chaff)monga mankhusu a pamapiri...Yes 17:13koma mankhusu adzatentha ndi moto...Mat 3:12[onaninso: mungu]

MANKHWALA (medicine)ngati mankhwala abwino...Miy 17:22mafuta a mankhwala pang’ono...Gen 43:11

MANOWA (Manoah) wa fuko la Adani; bambo ake a Samsoni...Ower 13:1-25

MANTHA (awe)ponse pali anthu achite mantha...Mas 33:8koma mtima wanga uchite mantha...Mas 119:161

MANTHA (fear)ndikukuchititsa mantha...Deut 2:25wodabwitsa ndi lochititsa mantha...Deut 28:58uyesa chabe mantha...Yob 15:4simudzachita nako mantha...Yob 33:7aseka mantha osaopsedwa...Yob 39:22akuchititseni mantha...Yes 8:13atsalawo achite mantha...1 Tim 5:20sanatipatsa Mzimu wa mantha...2 Tim 1:7mulibe mantha mchikondi...1 Yoh 4:18muli amantha bwanji...Mat 8:26mantha ndi kunjenjemera...Mas 55:5m’Ziyoni ali ndi mantha...Yes 33:14nandilanditsa m’mantha anga...Mas 34:4mantha ali nacho chilango...1 Yoh 4:18[onaninso: opa]

MANTHA (fearful)muli amantha bwanji...Mat 8:26[onaninso: opsa]

MANTHA (fears)nandilanditsa m’mantha anga...Mas 34:4chikondi changwiro chitaya kunja mantha...1 Yoh 4:18[onaninso: opsa]

MANTHA (sorrow)ndi mantha avumbuluka patsogolo pake...Yob 41:22[onaninso: chisoni, kulira, kupweteka, kusauka]

MANTHA (terror)ndi m’zipinda mantha...Deut 32:25

[onaninso: choopsa, kunjenjemera, opsa]

MANYAZI (dishonour)nachite manyazi iwo...Mas 40:14ndi mnzake zamanyazi...Aro 1:24ankachitana za manyazi...Aro 1:27ncha manyazi kuti mkazi...1 Akor 14:35kumachititsa manyazi...Aef 5:12chaulemu ndi china chamanyazi...Aro 9:21onaninso: mnyozo, peputsa, zopanda ulemu]

MANYAZI (dishonours)nchamanyazi kwa mwamuna...1 Akor 11:14

MANYAZI (shame)achitedi manyazi...Mas 83:17amachititsidwa manyazi...Mas 97:7kupirikitsidwa mwa manyazi...Mas 129:5zitsiru adzazichititsa manyazi...Miy 3:35yokolola amachititsa manyazi...Miy 10:5tikuchita manyazi...Yer 51:51kuti ukhale manyazi...Hos 4:7iyeyo sadzachita manyazi...Aro 9:33iye sadzachita manyazi...Aro 10:11kuti ndikuchititseni manyazi...1 Akor 6:5kuchita nazo manyazi…Afil 3:19

MAONEKEDWE A THUPI (bodily)anatsika ndi maonekedwe a thupi...Luk 3:22koma maonekedwe a thupi lake...2 Akor 10:10

MAONEKEDWE (appearance)usayang’ane maonekedwe...1 Sam 16:7maonekedwe ao ada...Malio 4:8maonekedwe a nkhope...Luk 9:29poyang’ana maonekedwe...Yoh 7:24zooneka ndi maso…2 Akor 5:12mupenyerere zopenyeka pamaso...2 Akor 10:7popezedwa m’maonekedwe ngati...Afil 2:8kwinaku mauwo amaoneka...Akol 2:23kufikira maonekedwe a Ambuye...1 Tim 6:14tsopano m’maonekedwe a Ambuye...2 Tim 1:10ndi pa maonekedwe ake ndi ufumu wake...2 Tim 4:1amene anakonda maonekedwe ake...2 Tim 4:8ndi maonekedwe a ulemelero wa Mulungu...Tit 2:13maonekedwe ake akunga Lebano...Nyi 5:15kuonekera kwake kunali...Mat 28:3

MAONEKEDWE (countenance)maonekedwe ake akunga Lebano...Nyi 5:15[onaninso: kuoneka, nkhope]

MAONEKEDWE (form)ndi maonekedwe a thupi...Luk 3:22maonekedwe ake simunaona... Yoh 5:37maonekedwe a dziko ili apita...1 Akor 7:31pokhala nao maonekedwe a...Afil 2:6mupewe maonekedwe onse a choipa...1 Ates 5:22akukhala nao maonekedwe a...2 Tim 3:5

MAPANGA (caves)anthuwo anabisala m’mapanga...1 Sam 13:6anthu adzalowa m’mapanga...Yes 2:19ndi m’mapiri, ndi m’mapanga...Aheb 11:38

MAPANGANO (covenants)akaziwa ali mapangano awiri...Agal 4:24ndi ulemelero ndi mapangano...Aro 9:4

MAPAZI (feet)nagona kumapazi ake...Rut 3:14

Page 88: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi mapazi anga sanaterereka...2 Sam 22:37ndi mapazi a otsimphina...Yob 29:15zonse pansi pa mapazi ake...Mas 8:6alinganiza mapazi anga...Mas 18:33munapondetsa mapazi anga...Mas 31:8mapazi anga akadaterereka...Mas 73:2mapazi anga alinkuima...Mas 122:2mapazi ao athamangira zoipa...Miy 1:16mapazi ake aumirira kumanda...Miy 5:5fumbi la m’mapazi ako...Yes 49:23akongolatu pa mapiri mapazi...Yes 52:7malo a mapazi anga ulemerero...Yes 60:13mitambo ndiyo fumbi la mapazi ake...Nah 1:3mapazi ake adzaponda tsiku...Zek 14:4naimirira kumboyo, pa mapazi...Luk 7:38wakukhala pa mapazi a Ambuye...Luk 10:39kusambitsa mapazi a akuphunzira...Yoh 13:5nawaika pa mapazi a atumwi...Mac 4:35mapazi a iwo akulalikira uthenga...Aro 10:15anagonjetsa zonse pansi pa mapazi ake...1 Akor 15:27mutaziveka mapazi anu...Aef 6:15ndinagwa pa mapazi ake...Chiv 1:17pa mapazi ake kumlambira...Chiv 19:10[onaninso: miyendo, phazi]

MAPEMBEDZEDWE (religion)mapembedzedwe oyenera...Yak 1:27[onaninso: chipembedzero, kupembedza, wopembedza]

MAPEMPHERO (prayers)manja anu popemphera...Yes 1:15nkumanyengezera kunena mapemphero...Mat 23:14kukukumbukirani m’mapemphero...Akol 4:12mapemphero ake akhale opempha...1 Tim 2:1kanthu koletsa mapemphero...1 Pet 3:7kuti muthe kupemphera...1 Pet 4:7mapemphero a anthu...Chiv 5:8[onaninso: pembedzo]

MAPIKO (wings)kuthawira pansi pa mapiko ake...Rut 2:12nauluka msanga pa mapiko...Mas 18:10m’munsi mwa mapiko anu...Mas 36:7ndikadzitengera mapiko...Mas 139:9liyense anali ndi mapiko...Yes 6:2muli kuchiritsa m’mapiko mwake...Malak 4:2adapatsidwa mapiko awiri...Chiv 12:14

MAPIRI (hills)mapiri achikhalire...Gen 49:26ndilo dziko la mapiri...Deut 11:11chuma cha m’mapiri...Mas 95:4maso anga kumapiri...Mas 121:1mapiri asanakhazikike...Miy 8:26

MAPIRI (mountains)iyeyo adasendeza mapiri...Yob 9:5mapiri adzabweretsa...Mas 72:3kupambana mapiri...Mas 76:4mapiri asanabadwe...Mas 90:2mapiri amasungunuka...Mas 97:5mapiri aakulu adalumphalumpha...Mas 114:4chuma cha m’mapiri...Mas 121:1momwe mapiri amazingira...Mas 125:2mapiri azinga Yerusalemu...Mas 125:2mapiri asanakhazikike...Miy 8:25mapiri adzachoka ndi...Yes 54:10athawire ku mapiri...Mat 24:16ndikasendeza mapiri...1 Akor 13:2mapiri sanapezeke...Chiv 16:20

MAPWANDO (feasts)

malo olemekezeka pa mapwando...Luk 20:46ndiwo amaipitsa mapwando...Yuda 12[onaninso: zikondwerero]

MARA (Marah)dzina losankhidwa ndi Naomi...Rut 1:20chithando choyamba cha Israeli atangooloka nyanjayofiira...Num 33:8-9

MARAYA (cloak)zonsezi zidzatha ngati maraya...Mas 102:26[onaninso: mwinjiro]

MARAYA (robe)namfunda iye maraya a chibakuwa...Yoh 19:2[onaninso: mkanjo]

MARIA (Mary)Mai ake a Yesu...Mat 1:16Anayenderedwa ndi mngelo...Luk 1:26-38Anamuyendera Elizabeti ndi kupereka matamando kwaAmbuye...Luk 1:39-56Anabereka Yesu...Luk 2:6-20Anathawira ku Ejipito...Mat 2:13-18Anapita ku Yerusalemu ndi Yesu...Luk 2:41-52Yohane anapatsidwa ntchito yowasamalira...Yoh 19:25-27— mai a Yakobo ndi Yosefe, analipo pa kupachikidwa ndikuikidwa kwaYesu...Mat 27:55-61anamuona mpulumutsi woukitsidwayo, anakauza ophunzira akea Yesu...Mat 28:1-10— Magadalena; anatulutsidwa ziwanda zisanu ndi ziwiri;anathandiza utumikiwa Yesu...Luk 8:2,3analipo nthawi yompachika ndi kumuika mmanda Yesu...Mat27:55-61woyamba kumuona Ambuye woukitsidwayo...Marko16:1-10;Yoh 20:1-18— mlongo wake wa Marita ndi Lazaro; wokondedwa ndiYesu...Yoh 11:1-5analirira Lazaro...Yoh 11:19,20,28-33anadzodza Yesu ndi mafuta...Mat 26:6-13;Yoh 12:1-8anayamikiridwa ndi Yesu...Luk 10:38-42— Mai ake a Marko...Mac 12:12-17

MARITA (Martha)mlongo wake wa Maria ndi Lazaro, okondedwa ndi Yesu...Yoh11:1-5analimbitsa chikhulupiriro chake...Yoh 11:19-28anaonetsa kukoma mtima kwaYesu...Luk 10:38;Yoh 12:1,2anadzudzulidwa ndi Yesu modekha...Luk 10:39-42

MARKO (John Mark)Mwana wamwamuna wa Maria wa ku Yerusalemu;anayendera limodzi ndi Barnabasi ndi Paulo...Mac 12:12,25anamuleka Paulo ku Perga...Mac 13:13Barnabasi ndi Paulo analekana chifukwa cha iye...Mac15:37-40kenaka anayamikiridwa ndi Paulo...Akol 4:10;2 Tim 4:11mnzake wa Petro...1 Pet 5:13Wolemba buku lachiwiri la uthenga wabwino...Marko 1:1

MASA NDI MERIBA (Massah and Meribah)koyamba ku Refidimu, Aisraeli atangotuluka mu Ejipito...Eks17:1-7kachiwiri, m’Kadesi, patatha zaka 40...Num 20:1-13

MASALIMO (psalms)ndi mau a Masalimo...Aef 5:19

MASAMBA (leaves)ndipo anasoka masamba a mkuyu...Gen 3:7palibe kanthu koma masamba okha...Mat 21:19

Page 89: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

masamba a mtengo ndiwo...Chiv 22:2[onaninso: siya]

MASANGALATSO (consolations)masangalatso a Mulungu akuchepa...Yob 15:11

MASANZI (vomit)choterereka pamasanzi...Yes 19:14wabwerera kumasanzi...2 Pet 2:22[onaninso: sanza]

MASAUTSO (adversities)m’mavuto ndi masautso...1 Sam 10:19mwaona masautso...Mas 31:7

MASAUTSO (adversity)ndi mazunzo...2 Mbir 15:6[onaninso: tsoka]

MASAUTSO (affliction)Mulungu wandipatsa ana mdziko la masautso...Gen 41:52[onaninso: chisautso, kuthyoka, kuzunza, kuzunzika, mazunzo,

nsauko, nthenda]

MASAYA (cheeks)masaya ako akukongola...Nyi 1:10masaya ake ali ngati timinda...Nyi 5:13masaya anga kwa ondimwetula ndevu...Yes 50:6

MASEDONIYA (Macedonia)Paulo analalikirako...Mac 16:9-17:14Paulo anakomana ndi mavuto kumeneko...2 Akor 7:5mipingo yake yoolowa manja...Aro 15:26;2 Akor 8:1-5

MASIKU ONSE (daily)nasanthula m’malembo m’masiku onse...Mac 17:11pamaso panga masiku onse palikulira...Yer 6:7[onaninso: tsiku ndi tsiku]

MASIKU (days)masiku anga afulumira koposa...Yob 7:6mundileke, pakuti masiku anga...Yob 7:16ngwa masiku owerengeka...Yob 14:1masiku a zaka zathu…Mas 90:10adzakuonjezera masiku ambiri...Miy 3:2usanene kodi bwanji masiku akale...Mlal 7:10asanadze masiku oipa...Mlal 12:1nawayesa masiku khumi...Dan 1:14Ambuye akadapanda kufupikitsa masikuwo...Marko 13:20kodi inu mudzamuutsa masiku atatu...Yoh 2:20musunga masiku ndi miyezi...Agal 4:10ndi kuona masiku abwino...1 Pet 3:10

MASO (eye)koma tsopano ndikupenyeni maso...Yob 42:5maso sakhuta m’kuona, ndi makutu sakhuta...Mlal 1:8pakuti adzaona maso ndi maso...Yes 52:8ndi mankhwala opaka m’maso mwako...Chiv 3:18[onaninso: diso]

MASO (eyes)maso anu adzatseguka...Gen 3:5ndipo mudzakhala maso athu...Num 10:31adapaka maso ake utoto...2 Maf 9:30maso a Chauta amayang’ana...2 Mbir 16:9maso anu ali ngati a munthu...Yob 10:4ndi maso anga adzamuona...Yob 19:27ndinali maso a akhungu...Yob 29:15maso ake achipenyetsetsa...Yob 39:29maso anga alinga kwa Yehova...Mas 25:15Maso a Yehova ali pa olungama...Mas 34:15m’maso mwanga mwada...Mas 69:3

koma udzapenya ndi maso...Mas 91:8ndikweza maso anga kumapiri...Mas 121:1maso anga agone...Mas 132:4maso anu anandipenya...Mas 139:16maso ako ayang’ane m’tsogolo...Miy 4:25koma maso a opusa...Miy 17:24ndani afiira maso...Miy 23:29maso a munthu sakhuta...Miy 27:20wanzeru maso ake ali m’mutu...Mlal 2:14kupenya kwa maso kuposa...Mlal 6:9maso ako akunga ankhunda...Nyi 1:15kuti maso anga aona mfumu...Yes 6:5ndi maso akhungu adzaona...Yes 29:18maso anga analephera...Yes 38:14maso anu sali pachoonadi kodi...Yer 5:3ali ndi maso koma saona...Yer 5:21ndidzaika maso anga pa iwo...Yer 24:6yodzala ndi maso...Ezek 1:18zinadzala ndi maso pozungulira...Ezek 10:12nyangayo idali ndi maso...Dan 7:20yooneka bwino pakati pa maso...Dan 8:5wa maso osalakwa...Hab 1:13koma maso anu ali odala...Mat 13:16anapaka thope m’maso mwanga...Yoh 9:15ndipo maso ao anawatseka...Mac 28:27mzimu watulo, maso kuti asapenye...Aro 11:8mukadakolowola maso anu...Agal 4:15chimene tidachiona m’maso mwathu...1 Yoh 1:1ndi chilakolako cha maso...1 Yoh 2:16maso ake ngati lawi la moto...Chiv 1:14mankhwala opaka m’maso...Chiv 3:18ndi maso asanu ndi awiri...Chiv 5:6kuichotsa pamaso pao...Chiv 21:4

MASO (face)koma pomwepo maso ndi maso...1 Akor 13:12ndinatsutsana naye pamaso pake...Agal 2:11[onaninso: nkhope]

MASULA (loose)ndidzamasula mchuuno mwa...Yes 45:1chimene ukamasula pa dziko...Mat 16:19ananena nao, mmasuleni...Yoh 11:44mwandimasulira zondimanga...Mas 116:16

MASULA (washed)ndi magazi ake anatimasula...Chiv 1:5[onaninso: chapa, konkha, sambitsa, sambitsidwa, tsuka]

MATALALA (hail)ndidzavumbitsa mvumbi wa matalala...Eks 9:18kapena unapenya zosungiramo matalala...Yob 38:22aponya matalala ake ngati...Mas 147:17ndipo matalala adzachotsa pothawira...Yes 28:17anatsika kumwamba matalala...Chiv 16:21

MATALALA (snow)ndidzakhala wa mbu woposa matalala...Mas 51:7zidzayera ngati matalala...Yes 1:18ndi chovala chake choyeretsedwa ngati matalala...Mat 28:3[onaninso: chipale chofewa]

MATANIYA (Mattaniah)dzina lenileni la mfumu Zedekiya...2 Maf 24:17

MATANTHWE (rocks)matanthwe adang’ambika...Mat 27:51mapiri ndi matanthwe...Chiv 6:16

MATAYA (generous)mtima wa mataya udzalemera...Miy 11:25mwini diso la mataya adzadala...Miy 22:9

Page 90: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: mfulu]

MATEYU (Matthew)anakhala wotsatira wa Yesu...Mat 9:9anasankhidwa kukhala m’modzi wa khumi ndi awiri aja...Mat10:2,3wotchedwa Levi, mwana wa Alifeyo...Marko 2:14wolemba buku loyamba la uthenga wabwino

MATHERO (end)mundidziwitse mathero a moyo wanga...Mas 39:4ndidzazitsata mpaka kumathero...Mas 119:33ndidaneneratu zakumathero...Yes 46:10kuchokera kumathero adziko...Mat 12:42[onaninso: chimaliziro, chitsiriziro, itha, maliza,

matsiriziro,tsiriza]

MATHERO (ends)kumathero a dziko lapansi...Mat 12:42[onaninso: malekezero, matsiriziro]

MATIASI (Matthias)anasankhidwa pochita maere kuti alowe m’malo mwaYudasi...Mac 1:15-26

MATIRIRA (cling)ndi kummatirira iye pakuti iye ndiye moyo...Deu 30:20[onaninso: khudza, gwira]

MATIRIRA (clings)moyo wanga umamatira ndi fumbi...Mas 119:25[onaninso: kangamira]

MATSENGA (magic)akuchita zamatsenga anasonkhanitsa...Mac 19:19

MATSIRIZIRO (end)koma matsiriziro ake ndi...Miy 14:12ndani wakhazikitsa matsiriziro...Miy 30:4[onaninso: chimaliziro,chitsiriziro, itha, maliza, mathero,

tsiriza]

MATSIRIZIRO (ends)ndani wakhazikitso matsiriziro...Miy 30:4[onaninso: mathero, malekezero]

MATSUTSANO (arguments)mkamwa mwanga ndi matsutsano...Yob 23:4ndikugwetsa matsutsano...2 Akor 10:5

MATUPI (bodies)mupereke matupi anu...Aro 12:1matupi anu ali ziwalo za...1 Akor 6:15palinso matupi a...1 Akor 15:40ngati matupi a iwo okha...Aef 5:28

MAU (command)mverani mau anga...Yer 11:4[onaninso: lamula, uza]

MAU (word)ndi mau onse otuluka...Deut 8:3mauwa ali pafupifupi ndi inu...Deut 30:14ndasunga mau anu...Mas 119:11mau anu anandipatsa moyo...Mas 119:50mau anu ndiye nyali...Mas 119:105mau abwino amamsangalatsa...Miy 12:25mau onena panthawi yake...Miy 15:23mau amodzi olankhula moyenera...Miy 25:11mau alionse a Mulungu...Miy 30:5Ambuye atumiza mau...Yes 9:8mau a Mulungu wathu...Yes 40:8

mau amene sadzasinthika...Yes 45:23mau ochokera m’kamwa mwanga...Yes 55:11mau anu, Inu Chauta...Yer 20:9mau a iye mwini...Yer 23:36amodzi a mau anga adzazengerezekanso...Ezek 12:28mungonena mau okha...Mat 8:8mau alionse opanda pake...Mat 12:36mbeu zija ndi mau...Luk 8:11wamphamvu m’ntchito ndi m’mau...Luk 24:19amatchedwa dzina loti mau...Yoh 1:1mau aja adasanduka munthu...Yoh 1:14munthu akamvera mau anga...Yoh 8:51mau amene muli kumvawa...Yoh 14:24muziwapatula ndi mau ...Yoh 17:17nayamikira mau a Ambuye...Mac 13:48kulankhula mau olangiza...1 Akor 12:8ndi madzi ndiponso mau...Aef 5:26pakuwauza mau opatsa moyo...Afil 2:16mau a Khristu akhazikike...Akol 3:16m’mau a choonadi cha Uthenga Wabwino...1 Ates 1:5ntchito yonse ndi mau onse abwino...2 Ates 2:17ndi mau ake amphamvu...Aheb 1:3sadapindule nawo mau...Aheb 4:2mau a Mulungu ndi a moyo...Aheb 4:12muwalandire mofatsa mau...Yak 1:21akapanda kukhumudwa pa mau...Yak 3:2mbeuyi ndi mau a Mulungu...1 Pet 1:23kalelo Mulungu atanena mau...2 Pet 3:5munthu akamasunga mau...1 Yoh 2:5tisakonde ndi mau...1 Yoh 3:18dzina lake Mau a Mulungu...Chiv 19:13

MAU (message)pakuti mau a mtanda...1 Akor 1:18[onaninso: uthenga]

MAU (words)imvani mau anga...Mas 5:1mau anga ndi maganizo...Mas 19:14mau anu ndi otsekemera...Mas 119:103labadirani mau a mkamwa mwanga...Miy 7:24mau a anzeru akunga zisonga...Mlal 12:11ndaika mau anga mkamwa...Yes 51:16mukani nao mau...Hos 14:2mau anga samchitira zokoma...Mik 2:7mau anga sadzatha...Mat 24:35ndi mau ogwira mtima...Luk 4:22mau amene ndalankhula...Yoh 6:63muli nao mau a moyowosatha...Yoh 6:68mau aja a Ambuye Yesu...Mac 20:35si mu nzeru ya mau...1 Akor 1:17amene akumva mau a chinenero...Chiv 1:3amene asunga mau a chinenero...Chiv 22:7

MAULAMULIRO (powers)atavula maukulu ndi maulamuliro...Akol 2:15[onaninso: mphamvu]

MAUNYOLO (chains)kumanga maufumu ao ndi maunyolo...Mas 149:8ndipo maunyolo anagwa...Mac 12:7[onaninso: ndende, nkhata, nsinga, zomangira]

MAUTA (bows)mauta amphamvu...1 Sam 2:4

MAVUTO (distress)tsiku la mavuto anga...Gen 35:3[onaninso: chisauko, chivuto, nsauko, nsautso, opsa, psinjika,saukira, sautsika]

MAWERE (breasts)

Page 91: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mawere ake akukwanire nthawi...Miy 5:19mawere ako awiri akunga...Nyi 4:5[onaninso: mabere]

MAWERENGEDWE A MAFUKO A MAKOLO (genealogies)nkhani zachabe ndi mawerengedwe a mafuko a makolo...1 Tim1:4

MAWINDO (windows)akusunzumira m’mawindo...Nyi 2:9yatifikira kudzera m’mawindo...Yer 9:21munali mawindo oyang’ana...Yes 6:2[onaninso: mazenera]

MAYANJANO (company)mayanjano oipa aipsa...1 Akor 15:33kuti musayanjane naye...2 Ates 3:14[onaninso: khamu, unyinji]

MAYANKHO (answers)olemera amayankha...Miy 18:23[onaninso: bwezera, vomera]

MAYENDEDWE (ways)adziwa mayendedwe a olungama...Mas 1:6ndidana nao mayendedwe onse...Mas 119:104[onaninso: njira]

MAZENERA (windows)ngati sindikutsegulirani mazenera a kumwamba...Mal 3:10[onaninso: mawindo]

MAZIKO (foundation)amene adzamange maziko...Yos 6:26umene Chauta adamanga maziko...Mas 87:1ndiwo maziko a mpando wachifumu...Mas 89:14mudaika maziko a dziko lapansi...Mas 102:25olungama ndiwo maziko osatha...Miy 10:25naika maziko pa thanthwe...Luk 6:48panthaka, osakumba maziko...Luk 6:49ndidakhazika maziko monga...1 Akor 3:10pajatu palibe maziko enanso...1 Akor 3:11maziko olimba, amene Mulungu...2 Tim 2:19kuphunzitsa zomwe zili ngati maziko...Aheb 6:1maziko aja omwe linga la mzindawo...Chiv 21:19

MAZIKO (foundations)muja ndinaika maziko a dziko lapansi...Yob 38:4akapasuka maziko wolungama...Mas 11:3anakhazika dziko lapansi pa maziko...Mas 104:5udzautsa maziko a mibadwo...Yes 58:12maziko a linga la mzinda...Chiv 21:19

MBADWO (generation)iwo ndiwo mbadwo wopulukira...Deut 32:5mbadwo wa oongoka mtima...Mas 112:2mbadwo wina udzalemekezera ntchito...Mas 145:4mbadwo wotembereredwa atate ao...Miy 30:11pali mbadwo wodziyesa woyera...Miy 30:12mbadwo wina upita, mbadwo...Mlal 1:4mbadwo uwu sudzatha kuchoka...Mat 24:34mbadwo uno wokhotakhota...Mac 2:40[onaninso: akubadwa, mibadwo]

MBALA (thief)pakuona mbala uvomerezana...Mas 50:18anthu sanyoza mbala ikaba...Miy 6:30woyenda ndi mbala ada moyo...Miy 29:24monga mbala ili ndi manyazi...Yer 2:26akulowera pawindo ngati mbala...Yow 2:9akadadziwa nthawi yiti mbala ikudza...Mat 24:43kumene mbala siziyandikira...Luk 12:33

koma chifukwa anali mbala...Yoh 12:6la Ambuye lidzadza ngati mbala...2 Pet 3:10tsono ndidzafika ngati mbala...Chiv 3:3[onaninso: wakuba]

MBALAME (bird)mafanidwe a mbalame iri yonse...Deut 4:17udzasewera nayo ngati mbalame...Yob 41:5phiri lanu ngati mbalame...Mas 11:1unaonjoka ngati mbalame...Mas 124:7msampha pamaso pa mbalame...Miy 1:17mbalame ku dzanj ala msodzi...Miy 6:5amtsata monga mbalame...Miy 7:23monga mbalame yosochera...Miy 27:8pakuti mbalame ya mlengalenga...Mlal 10:20nanyamuka polira mbalame...Mlal 12:4ngati mbalame zoyendayenda...Yes 16:2ndiitana mbalame yolusa...Yes 46:11ndi kuchoka ngati mbalame...Hos 9:11ngati mbalame ya ku Aigupto...Hos 11:11kodi mbalame idzakodwa...Amo 3:5nyama ndi wa mbalamenso...Yak 3:7ndi mosungiramo mbalamenso...Chiv 18:2

MBALAME (birds)ndipo mbalame zidzadya mnofu wako...Gen 40:19m’mwemo mbalame zimanga zisa zawo...Mas 104:17ndi mbalame zikodwa mumsampha...Mlal 9:12yang’anirani mbalame zakumwamba...Mat 6:26ndi mbalame zam’mlengalenga zisa zao...Mat 8:20

MBALE (brother)anali bwenzi langa kapena mbale wanga...Mas 35:14ukhala nuneneza mbale wako...Mas 50:20mbale wako anabadwira...Miy 17:17kupembedza mbale utamchimwira...Miy 18:19alibe mwana ngakhale mbale...Mlal 4:8musakhulupirire yense mbale wake...Yer 9:4mbale adzapereka mbale wake...Mat 10:21mbale wanga adzandichimwira...Mat 18:21uzani mbale wanga agawane...Luk 12:13uweruziranji mbale wako...Aro 14:10mbale anena mlandu ndi mbale ...1 Akor 6:6ndiye mbale amene Khristu anamfera...1 Akor 8:11mbale wokondedwa...Fil 16amene akonda mbale wake...1 Yoh 3:12namupha mbale wake...1 Yoh 2:10wakudana ndi mbale wake...1 Yoh 3:15akaona mbale wake alikuchimwa...1Yoh 5:16ine Yohane, mbale wanu...Chiv 1:9

MBALE (brother’s)kali m’diso la mbale...Mat 7:3

MBALE YA ZOFUNIKA (censer)anatenga yense mbale yake ya zofunika...Lev 10:1aliyense ali ndi mbale yake ya zofunika...Ezek 8:11okhala nayo mbale ya zofunika...Aheb 9:4mngeloyo anatenga mbale ya zofunika...Chiv 8:5

MBALE (bowls)alonga dzanja lake m’mbale...Miy 19:24ngakhale m’mbale ya golidi...Mlal 12:6ndi mbale za golidi...Chiv 5:8mbale zisanu ndi ziwiri...Chiv 16:1natsanulira m’mbale...Chiv 16:2akukhala nazo mbale zisanu...Chiv 21:9

MBANDAKUCHA (morning)kuwala kwa mbandakucha...Yob 41:18kuoneka ngati mbandakucha...Ny 6:10mwana wa mbandakucha...Yes 14:12

Page 92: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

konse ngati mbandakucha...Hos 6:3[onaninso: mmawa]

MBENDERA (banners)tidzakweza mbendera...Mas 20:5aika mbendera zao zikhale...Mas 74:4ngati nkhondo ndi mbendera...Nyi 6:4

MBEU ZOKOMETSERA CHAKUDYA (anise)ndi cha timbeu tokometsera chakudya...Mat 23:23

MBEU (descendants)mbeu yonse ya Israeli...Yes 45:25tiri mbeu ya Abrahamu...Yoh 8:33[onaninso: mbumba]

MBEU (seed)zidzaitanidwa mbeu zako...Gen 21:12chotero mbeu yopatulika...Yes 6:13Iye adzaona mbeu yake...Yes 53:10mbeu yopanda pake...Yer 2:21mbeu zija ndi mau a Mulungu...Luk 8:11sanatisiyira ife mbeu...Aro 9:29mbeu iliyonse m’mera...1 Akor 15:38Abrahamu ndi kwa mbeu...Agal 3:16muli mbeu ya Abrahamu...Agal 3:29wochekera m’mbeu ya Davide...2 Tim 2:8m’mbeu yosatha kuwonongeka...1 Pet 1:23mbeu yake ikhala mwa iye...1 Yoh 3:9

MBIDZI (donkeys)mbidzi zipherako ludzu lawo...Mas 104:11mbidzi zinaima pamapiri oti se...Yer 14:6[onaninso: abulu]

MBIYA (basket)ndi kuivundikira m’mbiya...Mat 5:15[onaninso: mtanga]

MBIYA (pitchers)ndi mbiya zopanda kanthu...Ower 7:16[onaninso: miphika]

MBIYA (pot)siliva ali ndi mbiya...Miy 17:3momwemo munali mbiya ya golidi...Aheb 9:4[onaninso: mtsuko, nkhali]

MBONI (eye witnesses)iwo amene anakhala mboni...Luk 1:2

MBONI (witness)Mulungu ndiye mboni...Gen 31:50mboni yanga ili kumwamba...Yob 16:19mboni yanga yokhulupirika...Mas 89:37mboni yokhulupirika sinama...Miy 14:5akhale mboni yanga...Yes 55:4akhale mboni yoona...Yer 42:5adabwera ngati mboni...Yoh 1:7pokhapokha patapezeka mboni...Deut 17:6ndidapeza mboni zokhulupirika...Yes 8:2ndinu mboni zanga...Yes 43:10pamaso pa mboni...1Tim 6:12pozungulira pali mboni...Aheb 12:1ndidzatuma mboni zanga...Chiv 11:3[onaninso: umboni]

MBUMBA (descendants)inu nonse mbumba ya Yakobo...Mas 22:23mbumba zake zidzalandira...Mas 25:13[onaninso: mbeu]

MBUSA (shepherd)mbusa wa anthu anga...2 Sam 5:2Chauta ndiye mbusa wanga...Mas 23:1kuti adzakhale mbusa...Mas 78:71zake ngati mbusa...Yes 40:11iye uja ndi mbusa...Yes 44:28koma ine pokhala mbusa...Yer 17:16poti palibe mbusa...Ezek 34:5ndidzaziika mbusa wanga...Ezek 34:23monga mbusa amangotolako...Amo 3:12tsoka kwa mbusa...Zek 11:17ndidzapha mbusa...Mat 26:31ndine mbusa wabwino...Yoh 10:11ndiye mbusa wamkulu...Aheb 13:20pamene mbusa wamkulu...1 Pet 5:4adzakhala mbusa wao...Chiv 7:17[onaninso: weta]

MBUYE (master)Abrahamu mbuye wake...Gen 24:9alingane ndi mbuye wake...Mat 10:25saposa mbuye wake...Yoh 15:20zedi kwa mbuye wake...2 Tim 2:21

MBUZI (goats)kapena kumwa mwazi wa mbuzi...Mas 50:13mbusa alekanitsa nkhosa ndi mbuzi...Mat 25:32mwa mwazi wa mbuzi ndi ana a ng’ombe...Aheb 9:12zamphongo ndi mbuzi...Aheb 10:4

MBWEBWE (divination)anali ndi mzimu wambwebwe...Mac 16:16[onaninso: mlauli, kulosa, ombeza]

MBWEBWE (mute)mbwebwe amene satha kulankhula...Mas 38:13ndine mbwebwe, nditseka...Mas 39:9[onaninso: wosalankhula]

MCHENGA (sand)zochuluka ngati mchenga...Gen 32:12mchenga wonse wamnyanja...Yob 6:3ambiri kuposa mchenga...Yes 10:22achuluke ngati mchenga...Mas 139:18yosawerengeka ngati mchenga...Aheb 11:12

MCHERE (salt)zakudya uzitsire mchere...Lev 2:13ndinu mchere wa dziko...Mat 24:6ngati mcherewo watha mphamvu...Marko 13:7

MCHIU (almond)mchiu nudzaphuka...Mlal 12:5[onaninso: katungurume]

MDALITSO (blessing)nukhale iwe mdalitso...Gen 12:2zikhale mdalitso...Ezek 34:26ndikusiya mdalitso...Yow 2:14mudzakhala chodalitsa...Zek 8:18

MDANI (adversary)angasanduke mdani wathu...1 Sam 29:4adani athuwa...Mas 74:10adani adamulanda...Mali 1:10pakati pa ine ndi mdani...Luk 18:3adani athu asapeze…1 Tim 5:14mdani wanu satana...1 Pet 5:8

MDANI (enemy)ndidzakhala mdani wa adani ako...Eks. 23:22bwanji mukundiyesa mdani...Yob 13:24

Page 93: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

iye akundiyesa mdani wake...Yob 33:10kumulanda zinthu mdani wanga...Mas 7:4kuti muwaletse mdani...Mas 8:2mdani wanga sadandipambane...Mas 41:11akadakhala mdani wanga...Mas 55:12mdani wandilondola wavimviniza...Mas 143:3mdani wako akakhala ndi njala...Miy 25:21mdani wako ngakhale akumpsompsone...Miy 27:6ndakulasa ndi bala la mdani...Yer 30:14usandiseka mdani wangawe...Mika 7:8ndi kudana ndi mdani wako...Mat 5:43mdani wotsiriza kumthetsa mphamvu...1Akor 15:26monga ndasanduka mdani wanu...Agal 4:16musamuwone ngati mdani...2 Ates 3:15amazisandutsa mdani wa Mulungu...Yak 4:4

MDIMA (dark)adzakhala mu mdima waukuru...1 Maf 8:12malo a dziko la mdima...Yes 45:19wandikhalitsa mu mdima...Mali 3:6chimene ndikuuzani inu mumdima...Mat 10:27nyali younikira malo a mdima...2 Pet 1:19[onaninso: ida]

MDIMA (darkness)ndi mdimawo anatcha usiku...Gen 1:5Yehova adzawaunika mumdima...2 Sam 22:29aweruza kodi mwa mdima wa bii...Yob 22:13iwo akukhala mu mdima...Mas 107:10ungakhale mdima sudetsa pamaso...Mas 139:12anthu amene amayenda mumdima...Yes 9:2ndidzawalitsa mdima...Yes 42:16ndi mdima wa bii mitundu ya anthu...Yes 60:2kapena dziko la mdima woti bii...Yer 2:31nasanduliza mdima wa ndiweyani...Amo 5:8adzatayidwa ku mdima wakunja...Mat 8:12ulamuliro wa mdima ndi wanu...Luk 22:53anthu anakonda mdima...Yoh 3:19woyenda mumdima sadziwa...Yoh 12:35kale munali mumdima...Aef 5:8dziko lapansi a mdima uno...Aef 6:12ku ulamuliro wa mdima...Akol 1:13sitiri a usiku kapena a mdima...1 Ates 5:5ndipakuda bii, ndi mdima...Aheb 12:18anakuitanani muturuke mumdima...1 Pet 2:9mdima wakuda bii uwasungikira...2 Pet 2:17mwa Iye monse mulibe mdima...1Yoh 1:5ndipo tiyenda mumdima...1 Yoh 1:6mdima uli kupita...1Yoh 2:8mdima wakuda bii unazisungikira...Yud 13

MDIMA (dim)diso lake silinachita mdima...Deut 34:7[onaninso: chidima]

MDINDO (eunuch)ku Aitiopiya, mdindo...Mac 8:27

MDULIDWE (circumcision)iye chipangano cha mdulidwe...Mac 7:8kapena suli mdulidwe umene...Aro 2:28ndipo mdulidwe uli wa mtima...Aro 2:29adzawayesa a mdulidwe olungama...Aro 3:30Khristu adakhala mtumiki wa mdulidwe...Aro 15:8mdulidwe ulibe kanthu...1 Akor 7:19uthenga wabwino wa mdulidwe...Agal 2:7kapena mdulidwe kapena kusadulidwa...Agal 5:6pakuti ife ndife mdulidwe...Afil 3:3ndi mdulidwe wosachitika ndi manja...Akol 2:11makamaka iwo a ku mdulidwe...Tit 1:10

MDZAKAZI (bondwoman)

chotsa mdzakazi uyo...Gen 21:10wobadwa mwa mdzakazi...Agal 4:22

MDZAKAZI (maidservant)ndine Rute mdzakazi wanu...Rut 3:9mundipulumutse ine mwana wa mdzakazi...Mas 86:16onani mdzakazi wa Ambuye...Luk 1:38umphawi wa mdzakazi wake...Luk 1:48

MEDI (Medes, Media)mbali ya ufumu wa Medo-Persiya...Est 1:19Israeli anatengeredwako ukapolo...2 Maf 17:6Anagwetsa Babulo...Dan 5:30,31Daniele anakwezedwa mu ufumu wake...Dan 6:1-28Koresi mfumu yake inalola Ayuda abwerere kwao...2 Mbir36:22,23anathandizira kugwa kwa Babulo...Yes 13:17-19

MEFIBOSETI (Mephibosheth)mwana wa mfumu Saulo, 2 Sam 21:8— Chidzukulu cha mfumu Saulo, mwana wolumala waYonatani...2 Sam 4:4-6anafunidwa ndi kupatsidwa ulemu ndi Davide...2 Sam 9:1-13Analeredwa ndi Ziba...2 Sam 16:1-4Kenaka anafotokozera za iye mwini kwa Davide...2 Sam19:24-30Anasungidwa ndi Davide...2 Sam 21:7mwana wa mfumu Saulo...2 Sam 21:8

MEGIDO (Megiddo)mzinda wa Akanani; malo omenyanirapo nkhondo...Owe5:19-21;2 Maf 23:29,30unamangiridwa malinga a chitetezo ndi mfumu Solomo...1 Maf9:15malo amene nkhondo ya Armagedo ikhozakudzachitikira...Chiv 16:16

MELITA (Malta)malo omwe chombo chinamuswekera Paulo...Mac 28:1-8

MELKIZEDEKI (Melchizedek)wansembe komanso mfumu ya ku Salemu...Gen 14:18-20mtundu wa unsembe wosatha wa Khristu...Aheb 7:1-22

MEMFISI (Memphis or Noph)boma lakale lalikulu la Ejipito...Hos 9:6linaneneredwa uneneri ndi Yesaya...Yes 19:13Ayuda anathawirako...Yer 44:1Anakanidwa ndi aneneri...Yer 46:19

MENAHEMU (Menahem)mfumu ya nkhanza ya Israeli...2 Maf 15:14-18

MENYA (beat)udzammenya ndi ntyole...Miy 23:14sudzanyamula lupanga kumenyana...Yes 2:4ukumamenya ena...Mat 26:67[onaninso: guguda, panda, puntha]

MENYA (fight)Chauta ndiye amene akumenyereni...Eks 14:14Mulungu wathu adzatimenyera...Neh 4:20anyamata anga atamenya...Yoh 18:36uzimenya nkhondo yabwino...1Tim 6:12m’chifukwa chake mumamenyana...Yak 4:2[onaninso: nkhondo]

MENYA (fights)Chauta ndiye akumenyereni nkhondo...Yos 23:10poti mukum’menyera nkhondo...1 Sam 25:28[onaninso: nkhondo]

Page 94: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MENYA (strike)menya wonyoza ndipo achibwana adzachenjera...Miy 19:25[onaninso: kantha, menya, panda, tentha, wamba]

MENYA (struck)ndinakwiya ndi kummenya iye...Yes 57:17[onaninso: kantha, panda]

MENYEDWA (beaten)katatu ndinamenyedwa ndi...2 Akor 11:25[onaninso: bwanyulidwa, kwapula, kwapulidwa]

MERABI (Merab)Mwana wamkazi wamkulu wa mfumu Saulo...1 Sam 14:49Saulo analonjeza Davide kuti adzamkwatira koma adamperekakwa Adiriyelo1 Sam 18:17-19

MERARI (Merari)Mwana wachitatu wa Levi...Gen 46:11— zidzukulu zake zotchedwa Amerani. Ntchito zao zaMuchihema...Num 3:35-37Mizinda inapatsidwa kwa iwo...Yos 21:7,34-40Ntchito za mkachisi...1 Mbir 26:10-19Anamthandiza Ezara atachoka ku ukapolo...Ezara 8:18,19

MERETSERA (spring)tsiku ilo ndidzameretsera nyumba...Ezek 29:21[onaninso: kasupe, oneka, phukira]

MERIBAALA (Merib-Baal)Dzina lina la Mefiboseti...1 Mbir 8:34

MERODAKI (Merodach)Mulungu wamkulu wa Ababulo...Yer 50:2kapenanso wotchedwa Beli...Yes 46:1

MERODAKI-BALADANI (Merodach-Baladan)Anatumiza akazembe kwa Hezekiya...Yes 39:1-8Wotchedwanso Berodaki-Baladani...2 Maf 20:12

MESEKI (Meshech)Mwana wa Yafeti...Gen 10:2Zidzukulu zake zinanenedwa mu uneneri...Ezek27:13;32:26;38:2,3

MESIYA (Messiah)Tapeza ife Mesiya...Yoh 1:41ndidziwa kuti Mesiya...Yoh 4:25[onaninso: wodzodzedwayo]

MESOPOTAMIYA (Mesopotamia)Kwawo kwa abale ake a Abrahamu...Gen 24:4,10,15Wotchedwa Padani Aramu ndi Siriya...Gen 25:20;31:20,24Israeli anakhala kapolo...Ower 3:8-10Ayuda ochokera kumeneku analiponso pa tsiku laPentekoste...Mac 2:9

METUSELA (Methuselah)Munthu wamkulu kwambiri pa mbiri ya dziko...Gen 5:27

MEZA (swallow)chinsomba chachikulu chimeze Yona...Yon 1:17akukuntha udzudzu koma ngamila mummeza...Mat 23:24[onaninso: namzeze]

MFARISI (Pharisee)winayo Mfarisi ndi mnzake...Luk 18:10ine ndine Mfarisi...Mac 23:6

MFULU (generous)koma mfulu aganizira zaufulu...Yes 32:8

[onaninso: mataya]

MFUMU (counselor)palibe mfumu mwa iwe kodi...Mika 4:9[onaninso: phungu]

MFUMUKAZI (queen)mfumukazi Vasiti...Est 1:9lamanja kwaima mfumukazi...Mas 45:9mfumukazi ya kumwamba...Ezek 44:17mfumukazi yakum’mwera ija...Mat 12:42m’banja la mfumukazi...Mac 8:27

MHELENE (Greek)kuyambira Myuda ndiponso Mhelene...Aro 1:16muno mulibe Myuda kapena Mhekene...Agal 3:28[onaninso: Griki]

MIBADWO (ages)anthu m’mibadwo ina...Aef 3:5[onaninso: nthawi, nyengo]

MIBADWO (generations)ndidzawakumbutsa dzina lanu m’mibadwo...Mas 145:17chilemekezo chanu ku mibadwo...Mas 79:13anawalamulira mibadwo zikwi...Mas 105:8anthu a mibadwo yonse adzanditcha...Luk 1:48

MICHEMBO (holes)nkhandwe zili ndi michembo...Mat 8:20

MIDIYANI (Midian)mwana wa Abrahamu kudzera mwa Ketura...Gen 25:1-4— dera ku chipululu cha ku Arabia chodzala ndiAmidiyani...Gen 25:6; Eks 2:15

MIGWALANGWA (palm)migwalangwa makumi asanu ndi awiri...Eks 15:27[onaninso: kanjedza]

MIINJIRO (robes)kuyendayenda ovala miinjiro...Luk 20:46[onaninso: zovala]

MIKA (Micah)Mneneri, nthawi ya Yesaya...Yes 1:1;Mik 1:1

MIKAELE (Michael)kalonga wamkulu...Dan 10:13,21anakangana ndi Satana…Yuda 9anamenyana ndi Chilombo...Chiv 12:7-9

MIKALA (Michal)mwana wamkazi wa mfumu Saulo...1 Sam 14:49anakonda ndi kukwatiwa ndi Davide...1 Sam 18:20-28anampulumutsa Davide kuchokera kwa Saulo...1 Sam 19:9-17anapatsidwa kwa Paliti...1 Sam 25:44Davide anamfuna kuchokera kwa Abineri...2 Sam 3:13-16adanyoza Davide nakhala ouma osabereka...2 Sam 6:16-23

MIKANGANO (contentions)amathetsa mikangano...Miy 18:18maina a makolo, mikangano...Tit 3:9[onaninso: ndeu]

MIKANGO (lions)moyo wanga uli pakati pa mikango...Mas 57:4anatseka pakamwa pa mikango...Aheb 11:33

MIKATE (loaves)koma mikate isanu ndi nsomba...Mat 14:17

Page 95: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

natenga mikateyo isanu ndi iwiri...Mat 15:36bwenzi, ndibwereke mikate...Luk 11:5chifukwa munadya mkate...Yoh 6:26

MIKAYA (Micaiah)Mneneri amene analosera za imfa ya Ahabu...1 Maf 22:8-28— anakhalapo nthawi ya Yeremiya...Yer 36:11-13

MIKIMASI (Michmash)malo omenyerana nkhondo ndi Afilisti...1 Sam 13:5,11,16,23malo a chigonjetso cha Yonatani...1 Sam 14:1-16

MIKOMBERO (wheels)adapinda mikombero ya...Eks 14:25kulira kwa mikombero ya...Yer 47:3maonekedwe a mikombero...Ezek 1:16[onaninso: njinga]

MIKUNGUZA (cedars)lithyola mitengo ya mikungudza...Mas 29:5mikungudza ya ku Lebano...Mas 104:16

MIKUYU (figs)mikuyu ikubereka zipatso...Nyi 2:13[onaninso: nkhuyu]

MILANDU (cases)dziko ladzala ndi milandu...Ezek 7:23

MILEME (bats)ku mfuko ndi ku mileme...Yes 2:20

MILETO (Miletus)Paulo anakomana ndi akulu ampingo a ku Efesopamenepa...Mac 20:15-38Paulo adamsiya Trofimo pamenepa...2 Tim 4:20

MILIKOMU (Milcom)fano lomwe solomoni ankapembedza...2 Maf 11:5guwa lake lidaonongedwa ndi Yosiya...2 Maf 23:12,13

MILIRI (plagues)ndidzatuma miliri yanga...Eks 9:14miliri yako ili kuti...Hos 13:14adzamuwonjezera Mulungu miliri...Chiv 22:18

MILO (Millo)linga la ku Yerusalemu...2 Sam 5:9wokonzedwera Solomoni...1 Maf 9:15unalimbitsidwa ndi Hezekiya...2 Mbir 32:5malo a imfa ya Yoasi...2 Maf 12:20,21

MILOMO (lips)ndine wa milomo yosadula...Eks 6:12Yehova adzadula milomo...Mas 12:3yosalankhula milomo yamabodza...Mas 31:18milomo ya olungama...Miy 10:21koma milomo yodziwa ndiye...Miy 20:15munthu wa milomo yonyansa...Yes 6:5uli pansi pa milomo yao...Aro 3:13ndi milomo ina ndidzalankhula nao...1 Akor 14:21milomo yake isalankhule chinyengo...1 Pet 3:10

MILUNGU (gods)ndi Mulungu wopambana milungu yonse ……...Deut 10:17amatsenga, milungu ya mnyumba...2 Maf 23:24akugamula mlandu milungu ya...Mas 82:1inu ndinu milungu, nonsenu ndinu...Mas 82:6anawatcha milungu anthu aja...Yoh 10:35yatitsikira milungu yooneka...Mac 14:11

MIMBA (belly)

uziyenda ndi pa mimba pako...Gen 3:14ndipo Yona anali m’mimba mwa...Yon 1:17pakuti monga Yona anali m’mimba...Mat 12:40Mulungu wawo ndiyo mimba yawo...Afil 3:19

MIMBA (womb)m’mimba mwako muli mitundu...Gen 25:23Mulungu anatseka mimba yake...1 Sam 1:5kukuumba m’mimba mwa mai...Yes 44:2dzina ndikadali m’mimba...Yes 49:1ndisanakulenge m’mimba mwa...Yer 1:5chodalitsika chipatso cha mimba yako...Luk 1:42yodala mimba imene inakubalani...Luk 11:27

MINDA (fields)m’minda musatuluke kanthu...Hab 3:17koma ndithu, taonani m’mindamu...Yoh 4:35[onaninso: kubusa]

MING’ALU (breaches)konzani ming’alu yake...Mas 60:2

MINGA (thorns)minga ndi mitula idzakubalira...Gen 3:18minga ndi misampha iri...Miy 22:5ponsepo panamera minga...Miy 24:31kuseka kwa chitsiru kuminga...Mlal 7:6ngati kakombo pakati pa minga...Nyi 2:2musabzale minga...Yer 4:3abzyala tirigu asenga minga...Yer 12:13koma zina zinagwa paminga...Mat 13:7atavara korona waminga...Yoh 19:5

MIPATUKO (divisions)oyambitsa mipatuko...Yud 19munthu woyambitsa mipatuko...Tit 3:10magawano, mipatuko ...Agal 5:20m’tseri mipatuko yotayikitsa...2 Pet 2:1[onaninso: patulana]

MIPESA (grapes)mipesa niphuka, inunkhira...Nyi 2:13[onaninso: mphesa]

MIPHIKA (pitchers)zikho ndi miphika...Marko 7:4[onaninso: mbiya]

MIPINGO (Churches)Kilikiya nakhazikitsa mipingo...Mac 15:41mipingo yonse ya Chikhristu...Aro 16:16zidagweranso mipingo ya Mulungu...1Ates 2:14ndikulembera mipingo isanu...Chiv 1:4ndi mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 1:20ndipo zithandize mipingo...Chiv 22:16

MIPIRINGIZO (bars)paja amalimbitsa mipiringizo ya...Mas 147:13ndidzathyola mipiringizo yake ya...Yes 45:2kudziko kumene mipiringizo inandisekera...Yon 2:6

MIRIYAMU (Miriam)mlongo wao wa Aroni ndi Mose...Num 26:59wosankhidwa ndi Mulungu; wotchedwa mneneri wamkazi...Eks15:20analangidwa chifukwa choukira...Num 12:1-6anaikidwa pa Kadesi...Num 20:1

MISAKI (Meshach)Dzina lopatsidwa kwa Misaele...Dan 1:7Anakwezedwa pa udindo waukulu...Dan 2:49Akhala wokhulupirika pamayeso...Dan 3:13-30

Page 96: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MISALA (madness)m’manja mwao ngati wamisala...1 Sam 21:13kudziwa nzeru ndi kudziwa misala...Mla 1: 17misala ili m’mitima yao akali...Mlal 9:3

MISAMPHA (snares)misampha ya imfa...Mas 18:5amanditchera misampha...Mas 38:12zoopsa, mbuna ndi misampha...Yes 24:17amatcha misampha...Yer 5:26

MITAMBO (clouds)mmawa mopanda mitambo...2 Sam 23:4mitambo idachucha madzi...Mas 77:17inu chisanu cha mbee ndi mitambo...Mas 148:8ndipo mitambo idagwetsa mvula...Miy 3:20wopenya mitambo sadzakolola...Mlal 11:4mwana wa munthu akubwera pa mitambo...Mat 24:30tidzakwatulidwa nawo pamodzi m’mitambo...1Ates 4:17mitambo yopanda madzi...Yud 12taonani adza ndi mitambo...Chiv 1:7

MITANGA (baskets)taonani mitanga iwiri ya nkhuyu...Yer 24:1mitanga khumi ndi iwiri yotsala...Mat 14:20[onaninso: malichero]

MITU YA NSANAMIRA (doorposts)kantha mitu ya nsanamira...Amo 9:1[onaninso: mphuthu]

MITUNDU (nation)ndi manenedwe ndi mitundu...Chiv 13:7[onaninso: mtundu]

MITUNDU MITUNDU (manifold)nzeru ya mitundu mitundu ya Mulungu...Aef 3:10chisomo cha mitundu mitundu cha Mulungu...1 Pet 4:10[onaninso: chuluka]

MITIMA (heart)zonse za maganizo a mitima yao...Gen 6:5mitima ya anthu idziwana...Miy 27:19[onaninso: mtima]

MITIMA (hearts)mumayesa maganizo ndi mitima...Mas 7:9mtima wanu ukhale ndi moyo...Mas 69:32 mitima yao ya iwo ofunsira Yehova...Mas 105:3adzabwezera mitima ya atate kwa ana...Mal 4:6adayesera mitima yao ndi chikhulupiriro...Mac 15:9udzasunga bwino mitima yanu...Afil 4:7uzikutsogolerani m’mitima mwanu...Akol 3:15

MITSINJE (brooks)dziko la mitsinje...Deut 8:7ngati madzi a timitsinje...Yob 6:15kukhumba mitsinje...Mas 42:1

MITSINJE (rivers)adasandutsa mitsinje...Mas 107:33misozi yambiri ngati mitsinje...Mas 119:136m’mbali mwa mitsinje ya...Mas 137:1mitsinje yonse imakathira...Mlal 1:7adzakhala malo a mitsinje...Yes 33:21ndikukupatsani mitsinje...Yes 43:19mitsinje ya madzi opatsa moyo...Yoh 7:38

MIUNI (firebrands)za miuni yofuka...Yes 7:4[onaninso: nsakali za moto]

MIVI (arrows)anatumiza mivi...2 Sam 22:15mivi yanu yandilowa...Mas 38:2mivi ya pauta...Mas 76:3akunga mivi m’dzanja...Mas 127:4mivi ya m’phodo...Malio 3:13mudatulutsa mivi m’phodo...Hab 3:9

MIVI (darts)kuzima nacho mivi yonse...Aef 6:16

MIYAMBA (heavens)kufikira miyamba kulibe...Yob 14:2miyamba ili ntchito ya manja anu...Aheb 1:10miyamba idzapita...2 Pet 3:10[onaninso: kumwamba, mlengalenga, thambo]

MIYENDO (feet)miyendo yao ichita liwiro...Aro 3:15[onaninso: mapazi, phazi]

MIYUNI (lights)kuthambo kukhale miyuni...Gen 1:14adalenga miyuni yaikulu...Mas 136:7Atate a zounikira zonse...Yak 1:17[onaninso: wala]

MIZA (drown)zilakolakozo zimamiza anthu...1 Tim 6:9

MIZAZA (flies)ndidzatumiza mizaza pa iwe...Eks 8:21[onaninso: ntchentche]

MIZINDA (cities)adaonongeratu mizinda imeneyi...Gen 19:25adzakonzanso mizinda imene...Yes 61:4mizinda yanu yoyera...Yes 64:10mizinda yanu idzakhala mabwinja...Yer 4:7mizinda ya maiko ena onse...Chiv 16:19achulukire mizindamo...Mas 72:16

MIZIPA (Mizpah)malo a pangano pakati pa Yakobo ndi Labani...Gen 31:44-53— Mzinda wa Benjamini;Aisraeli owawidwa mtima anasonkhana pamenepa...Yos18:21,26;Ower 20:1,3Samuele anawasonkhanitsa Aisraeli pamenepa...1 Sam7:5-16;10:17-25Kwawo kwa Gedaliya...2 Maf 25:23,25

MKAKA (milk)Yaele anampatsa mkaka...Owe 5:25kuli ngati uchi ndi mkaka...Nyi 4:11mudzagule vinyo ndi mkaka...Yes 55:1oyera kuposa mkaka...Malio 4:7kudzayenderera mkaka...Yow 3:18kukumwetsani mkaka...Aheb 5:12aliyense angomwa mkaka...Aheb 5:13amalirira mkaka...1 Pet 2:2

MKANGANO (contention)achitsiru amautsa mkangano...Miy 18:6[onaninso: kukangana]

MKANGO (lion)pansi nabwatana ngati mkango...Gen 49:9mundisaka ngati mkango...Yob 10:16ndipo mkango udzadya udzu...Yes 11:7ndidzakhala kwa Efraimu ngati mkango...Hos 5:14

Page 97: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MKANJO (robe)wandiveka mkanjo wachilungamo...Yes 61:10thamangani mukatenge mkanjo...Luk 15:22aliyense adapatsidwa mkanjo...Chiv 6:11[onaninso: maraya, mwinjiro]

MKATE (bread)anaturuka nawo mkate...Gen 14:18ndidzavumbitsira inu mkate...Eks 16:4sakhala wamoyo ndi mkate...Deut 8:3ndilibe mkate...1 Maf 17:12dziko la mkate...2 Maf 18:32mtima wake uchita nseru ndi mkate...Yob 33:20monga akudya mkate...Mas 14:4adzakhonzanso kupatsa mkate...Mas 78:20kudya mkate wosautsa...Mas 127:2ndidzawakhutitsa ndi mkate...Mas 132:15zikhala kwa iwo ngati mkate...Hos 9:4ndikusowa mkate m’malo mwanu...Amo 4:6miyala iyi isanduke mkate...Mat 4:3sadzakhala ndi moyo ndi mkate...Mat 4:4Yesu anatenga mkate...Mat 26:26asatenge mkate kapena thumba...Marko 6:8iye amene adzadya mkate...Luk 14:15akupatsani inu mkate...Yoh 6:32Ine ndine mkate wa...Yoh 6:48mkate umene tinyema...1 Akor 10:16anatenga mkate...1 Akor 11:23nthawi zonse mukadya mkate...1 Akor 11:26sitinadya mkate chabe...2 Ates 3:8

MKAZI WA LOTI (Lot’s wife)sanamvere, anasanduka chulu cha mchere...Gen 19:26chochitika choyenera kukumbukiridwa...Luk 17:32

MKAZI WAMASIYE (widow)adawachitira nkhanza akazi amasiye...Yob 24:21amapha akazi amasiye...Mas 94:6amachirikiza mkazi wamasiye...Mas 146:9milandu yao akazi amasiye...Yes 1:17wasanduka ngati mkazi wamasiye...Malio 1:1padafika mai wina wamasiye...Marko 12:42ngati mai wamasiye ali ndi ana...1 Tim 5:4m’gulu la azimai amasiye...1 Tim 5:9

MKAZI WADAMA (harlot)m’nyumba ya mkazi wadama...Yos 2:1mkazi wadama ndiye dzenje...Mlal 23:27amadzipereka kwa mkazi wadama...1 Akor 6:16Rahabu mkazi wadama...Aheb 11:31akukaweruzidwira mkazi wadama...Chiv 17:1

MKAZI (wife)amaphatikana ndi mkazi wake...Gen 2:24mkazi wabwino ali ngati...Miy 12:4wapeza mkazi wapeza...Miy 18:22mkazi wanzeru ndi wochokera...Miy 19:14mkazi amene umamkonda...Mlal 9:9ngati mkazi wapaunyamata...Yes 54:6kakwatire mkazi wachiwerewere...Hos 1:2kumeneko kuti apeze mkazi...Hos 12:12iwe ndi mkazi wako...Malak 2:15amene asudzula mkazi wake...Marko 10:11kumbukira za mkazi wa Loti...Luk 17:32mwini mkaziyo adzakhala uti...Luk 20:33wokonda mkazi wa iye...Aef 5:28akhale wa mkazi mmodzi...Tit 1:6mkazi wa mwanawankhosa...Chiv 21:9

MKAZI (woman)adzatchedwa mkazi...Gen 2:23mkazi wanzeru amamanga...Miy 14:1

mkazi woopa Chauta ndiye...Miy 31:30mkazi ndiye atsogola...Yer 31:22woyang’ana mkazi ndi kumkhumba...Mat 5:28wophunzira wina wamkazi...Mac 9:36adabadwa mwa mkazi...Agal 4:4koma mkazi amaonetsa...1 Akor 11:7kuti mkazi asaphunzitse...1 Tim 2:12mkaziyo ndiye adanyengedwa...1 Tim 2:14[onaninso: mai]

MKHALAPAKATI (mediator)Palibe mkhalapakati woti mkutiweruza...Yob 9:33wochita ntchito ya mkhalapakati...Agal 3:19mkhalapakati m’modzi yekha...1Tim 2:5[onaninso: nkhoswe]

MKHRISTU (christian)nkundisandutsa mkhristu...Mac 26:28akamva zowawa ngati mkhristu...1 Pet 4:16

MKONO (arm)thyolani mkono...Mas 10:15muli nao mkono...Mas 89:13mkono wake...Mas 98:1ndi mkono wake udzalamulira...Yes 40:10mkono wake unadzitengera...Yes 59:16ndipo mikono yanga...Yes 51:5zamphamvu ndi mkono...Luk 1:51[onaninso: dzanja]

MKONO (hand)taonani mkono wa Yehova sufupika...Yes 59:1[onaninso: dzanja, manja, pafupi, yandikira]

MKULU (captain)ngakhale mkulu...Miy 6:7

MKULU (elder)oneneza mkulu wa mpingo...1 Tim 5:19ine mkulu mnzao...1 Pet 5:1[onaninso: nkhalamba]

MKULU (prince)wakuika iwe ndani kuti ukhale mkulu...Eks 2:14ndipo munamupha Mkulu wa moyo...Mac 3:15monga mwa mkulu wa ulamuliro...Aef 2:2[onaninso: kalonga, mtsogoleri]

MKUNGUDZA (cedar)m’nyumba ya mikungudza...2 Sam 7:2adzakula ngati mkungudza...Mas 92:12mitanda ya nyumba zathu nja mikungudza...Nyi 1:17chindwi la mkati ndi mikungudza...Yer 22:14Asuri anali mkungudza...Ezek 31:3

MKUWA (brass)ndikhala mkuwa woomba...1 Akor 13:1ndi mapazi ake ngati mkuwa...Chiv 1:15

MKUWA (bronze)Mose anapanga njoka ya mkuwa...Num 21:9lidzakhala ngati mkuwa...Deut 28:23naphwanya njoka ija ya mkuwa...2 Maf 18:4mnofu wanga ndi mkuwa...Yob 6:12ndi mkuwa ngati mtengo woola...Yob 41:27adaswa zitseko za mkuwa...Mas 107:16m’malo mwa mkuwa ndidzatenga golide...Yes 60:17makoma a mkuwa pa dziko lonse...Yer 1:18ndidzakuyesa iwe linga la mkuwa...Yer 15:20ndi ufumu wina wachitatu wa mkuwa...Dan 2:39ndi ziboda zako zikhale za mkuwa...Mik 4:13ndiwo mapiri a mkuwa...Zek 6:1

Page 98: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MKUWA (copper)mapiri ake mukumbe mkuwa...Deut 8:9zotengera za mkuwa...Marko 7:4wosula mkuwa anandichitira...2 Tim 4:14

MKUYU (fig)adasoka masamba a mkuyu...Gen 3:7patsinde pa mpesa wake ndi mkuyu...1 Maf 4:25monga tsamba lofota pa mkuyu...Yes 34:4chinkana mkuyu suphuka...Hab 3:17kudzafuna chipatso pa mkuyu...Luk 13:7onani mkuyu ndi mitengo...Luk 21:29ndinakuona pansi pa mkuyu...Yoh 1:50kodi mkuyu ukhoza kubala...Yak 3:12monga mkuyu utaya nkhuyu...Chiv 6:13

MKWATI (bridegroom)monga mkwati avala nduwira...Yes 61:10monga mkwati akondwera ndi...Yes 62:5kulira nthawi imene mkwati...Mat 9:15pamene mkwati adzachotsedwa...Mat 9:15anaturuka kukakomana ndi mkwati...Mat 25:1pamene mkwati ali pamodzi nao...Marko 2:19mnzake wa mkwatiyo...Yoh 3:29

MKWATI (husband)pakuti iwe ndiwe mkwati wanga...Eks 4:25[onaninso: mwamuna]

MKWATIBWI (bride)ngati mkwatibwi...Yes 49:18amene ali naye mkwatibwi...Yoh 3:29ndidzakuonetsa mkwatibwi...Chiv 21:9mzimu ndi mkwatibwi anena...Chiv 22:17

MKWIYO (anger)chifukwa mkwiyo wawo...Gen 49:7kuti mkwiyo waukali...Num 25:4aleke mkwiyo wake...Deut 13:17kuti mkwiyo wake uchite...Deut 29:24pamene mkwiyo wa Yehova...Ower 10:7kuputa mkwiyo wanga...1 Maf 16:2pakuti mkwiyo wake...Mas 30:5muwatsanulire mkwiyo...Mas 69:24nabweza mkwiyo wake...Mas 78:38analambulira mkwiyo wake...Mas 78:50kukula kwa mkwiyo...Mas 90:11mkwiyo wake sudzakhala...Mas 103:9kumazimitsa mkwiyo...Miy 15:1mkwiyo woopsa...Miy 20:2chifukwa chake cha mkwiyo...Yes 5:25mkwiyo wanu wachoka...Yes 12:1pakuti mkwiyo ndi ukali...Yer 36:7ndidzakutumizirani mkwiyo...Ezek 7:3sasunga mkwiyo wake...Mik 7:18adzakhalitsa ndani pa mkwiyo...Nah 1:6mkwiyo wanga wayakira...Zek 10:3anawaunguza ndi mkwiyo...Marko 3:5ndi kupsa mtima ndi mkwiyo...Aef 4:31utauka mkwiyo...Mas 76:7[onaninso: kwiya]

MKWIYO (angry)ndipo utauka mkwiyo wanu...Mas 76:7[onaninso: kwiya]

MKWIYO (wrath)mkwiyo wa Chauta watsika...Num 16:46ndikadapanda kuopa mkwiyo...Deut 32:27mkwiyo umapha chitsiru...Yob 5:2mkwiyo wa anthu...Mas 76:10

mkwiyo wanu wandimiza...Mas 88:16ndi mkwiyo wanu woyaka...Mas 90:7pa tsiku la mkwiyo wao...Mas 110:5wanzeru amaupepesa mkwiyowo...Miy 16:14mkwiyo wa mfumu...Miy 19:12koma mkwiyo wa chitsiru...Miy 27:3mkwiyo umadzetsa nkhanza...Miy 27:4ndidzawamiza ndi mkwiyo...Hos 5:10anakulangizani kuthawa mkwiyo...Mat 3:7koma mkwiyo wa Mulungu ukhala...Yoh 3:36mkwiyo wa Mulungu...Aro 1:18ulikudziunjikira wekha mkwiyo...Aro 2:5chilamulo chichitira mkwiyo...Aro 4:15adaafuna kuonetsa mkwiyo...Aro 9:22mkwiyo wa Mulungu ndiwo...Aro 12:19kuopa mkwiyo wa Mulungu...Aro 13:5kaduka, mikwiyo, zilekanitso...2 Akor 12:20tinali oyenera mkwiyo...Aef 2:3kupsa mtima ndi mkwiyo...Aef 4:31wotipulumutsa ife ku mkwiyo...1 Ates 1:10amatipulumutsa ku mkwiyo ...1 Ates 2:16mopanda mkwiyo kapena...1 Tim 2:8wosaopa mkwiyo wa mfumu...Aheb 11:27ndi ku mkwiyo wa Mwanawankhosa...Chiv 6:16vinyo wa mkwiyo wa chigololo...Chiv 14:8mwa mkwiyo wa Mulungu...Chiv 14:19watsirizika mkwiyo wa Mulungu...Chiv 15:1vinyo wamkali wa mkwiyo wake...Chiv 16:19[onaninso: kuzaza, kwiya, udani, ukali]

MLALIKI (evangelist)kunyumba kwa mlaliki Filipo...Mac 21:8chita ntchito ya mlaliki wa uthenga...2 Tim 4:5

MLALIKI (preacher)nawa mawu a mlaliki...Mlal 1:1ngati palibe wina wolalikira...Aro 10:14kuti ndikakhale mlaliki...1 Tim 2:7mlaliki wa chilungamo...2 Pet 2:5

MLANDU (case)mlandu ukakulakani...Deut 1:17ndalongosola mlandu wanga...Yob 13:18ndikadalongosola mlandu wanga...Yob 23:4onetsani mlandu wanu...Yes 41:21Festo anafotokozera mfumuyo mlandu wake...Mac 25:14

MLAULI (divination)mau a mlauli ali m’milomo...Miy 16:10[onaninso: kulosa, mbwebwe, ombeza]

MLEMBI (clerk)mlembi wa mzindawo atawatontholetsa...Mac 19:35

MLENDO (alien)munali alendo...Deut 23:7andiyesa mlendo...Yob 19:15mlandu wa mlendo...Malak 3:5

MLENDO (foreigner)ine ndine mlendo wanu...Gen 23:4mulabadeko za ine mlendo...Rut 2:10koma mlendo yekhayu...Luk 17:18ndidzakhala mlendo kwa amene...1 Akor 14:11

MLENGALENGA (air)mbalame za m’mlengalenga...Gen 1:26ngati kupanda mlengalenga...1 Akor 9:26olankhula ku mlengalenga...1 Akor 14:9ulamuliro wa mlengalenga...Aef 2:2ndi Ambuye mumlengalenga...1 Ates 4:17mbale yake mumlengalenga...Chiv 16:17

Page 99: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: kumwamba]

MLENGALENGA (heavens)monga momwe mlengalenga ulili...Yes 55:9za mu mlengalenga zidzagwedezeka...Mat 24:29[onaninso: kumwamba, miyamba, thambo]

MLENGI (creator)ukumbukirenso mlengi wako...Mlal 12:1Mlengi wa malekezero a dziko...Yes 40:28[onaninso: wolenga]

MLENGI (maker)ali kuti Mulungu mlengi wanga...Yob 35:10munthu adzayang’ana kwa mlengi...Yes 17:7amene akangana ndi mlengi wake...Yes 45:9mlengi wako ndiye mwamuna wako...Yes 54:5Israeli waiwala mlengi wake...Hos 8:14[onaninso: womanga]

MLENJE (hunter)ndiwe mlenje wamkulu...Gen 10:9Esau adasanduka mlenje...Gen 25:27

MLEVI (levite)nanga Aroni mlevi mbale wako...Eks 4:14momwemonso mlevi, pofika pamenepo...Luk 10:32Yosefe wa fuko la levi...Mac 4:36

MLIRI (pestilence)ndiponso ku mliri...Mas 91:3mliri wogwa usiku...Mas 91:6kwake kudagwa mliri...Hab 3:5

MLIRI (plague)watsala mliri umodzi...Eks 11:1ndi mliriwo unaletseka...Mas 106:30[onaninso: cholanga]

MLONDA (watchman)mlonda angochezera ...Mas 127:1muike mlonda pakamwa...Mas 141:3iwe mlonda usikuwu...Yes 21:11ndakuika ukhale mlonda...Ezek 3:17

MLONGO (sister)ndiwe mlongo wanga...Yob 17:14mlongo wathu wamng’ono...Nyi 8:8mbale wanga ndi mlongo...Mat 12:50Febe, mlongo wathu...Aro 16:1mbaleyo kapena mlongoyo...1 Akor 7:15

MMAWA (morning)madzulo, mmawa ndi...Mas 55:17mmamawa patsiku lotsatira...Luk 24:1yowala mmamawa...Chiv 22:16[onaninso: mbandakucha]

MMISIRI WA MATABWA (carpenter)ameneneyu si mmisiri wa matabwa...Marko 6:3

MNAZARETE (Nazarene)adzatchedwa mnazarete...Mat 2:23

MNDANDANDA WA MAINA A MAKOLO ONSE (genealogy)motsatanatsatana maina a makolo onse...Mat 1:1wopanda mawerengedwe a chibadwidwe...Aheb 7:3

MNENERI (prophet)adzakhala ngati mneneri...Eks 7:1iye adzakutumizirani mneneri...Deut 18:15sadakhaleponso mneneri wina...Deut 34:10

ndathala ndekha mneneri...1 Maf 18:22kulibenso mneneri ndi m’modzi...Mas 74:9ndidakuika kuti ukhale mneneri...Yer 1:5ngati mneneri anyengedwa...Ezek 14:9mneneriyu nchitsiru...Hos 9:7ine sindine mneneri konse...Amo 7:14ndidzakutumizirani mneneri...Malak 4:5iye wakulandira mneneri pa dzina la mneneri...Mat 10:41mneneri amalemekezedwa kwina...Mat 13:57mneneri sangafere kwina...Luk 13:33iye anali mneneri amene...Luk 24:19ndiwe mneneri tikumuyembekeza...Yoh 1:21zoonadi ameneyu ndi mneneri...Yoh 6:14chidagwidwa pamodzi ndi mneneri...Chiv 19:20

MNG’ALU (clefts)ndi m’ming’alu ya m’nthaka...Yes 2:21m’ming’alu ya m’matanthwe...Yes 7:19

MNGELO WAMKULU (archangel)mau a mngelo wamkulu...1 Ates 4:16Mikaele mkulu wa angelo...Yuda 9

MNGELO (angel)mngelo wa Chauta...Gen 16:7mngelo amene wandiombola...Gen 48:16ndituma mngelo...Eks 23:20adaona mngelo...Num 22:23adazindikira kuti adalidi ndi mngelo...Ower 6:22Manowa adauza mngeloyo...Ower 13:17monga mngelo wa...1 Sam 29:9ndipo pamene mngelo...2 Sam 24:16mngelo wochokera...Yes 63:9adalimbana ndi mngelo...Hos 12:4adaima pamaso pa mngelo...Zek 3:3ngati mngelo wa...Zek 12:8mngelo wa Ambuye...Mat 1:20kuti mngelo wa Ambuye...Mat 28:2mngeloyo adaimirira...Luk 1:11mwadzidzidzi mngelo wa...Luk 2:9pamenepo mngelo wochokera...Luk 22:43nthawi zina mngelo...Yoh 5:4mngelo wolankhula naye...Yoh 5:4usiku mngelo wa Ambuye...Mac 5:19kudzera mwa mngelo uja...Mac 7:35pompo mngelo uja...Mac 7:35kulibe angelo...Mac 23:8kapena mngelo...Mac 23:9kunandibwerera mngelo...Mac 27:23ngati mngelo...2 Akor 11:14kaya ndi mngelo...Agal 1:8ndidaona mngelo...Chiv 5:2yake inali mngelo...Chiv 9:11ndidaona mngelo...Chiv 19:17ndatuma mngelo...Chiv 22:16[onaninso: mthenga]

MNOFU (flesh)mnofu wochokera ku mnofu...Gen 2:23[onaninso: anthu, thupi]

MNYOZO (contempt)atsanulira mnyozo pa akalonga...Yob 12:21ena kumanyazi ndi mnyozo wosatha...Dan 12:2[onaninso: kunyoza, kuyesedwa chabe]

MNYOZO (dishonour)lifesedwa m’mnyozo...1 Akor 15:43[onaninso: manyazi, peputsa, zopanda ulemu]

MNZAKO WA MLANDU (adversary)gwirizana naye mnzako wa mlandu...Mat 5:25

Page 100: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: mdani]

MNZAKO (fellow)m’modzi mwa antchito amnzake...Mat 18:28kumenya antchito amnzake...Mat 24:49iyeyu ndi wantchito mnzanga...2 Akor 8:23ndi ziwalo zinzathu...Aef 3:6Klemensi ndi antchito anzanga...Afil 4:3ndiwo antchito anzanga...Akol 4:11ndine kapolo mnzako...Chiv 19:10

MNZAKO (friend)Filemoni wokondedwayo ndi wantchito mnzathu...Fil 1mnzako ndi mnzake wa atate...Miy 27:10[onaninso: bwenzi]

MNZAKO (neigbour)mukonde mnzanu monga...Lev 19:18mnzako wokhala naye...Miy 27:10kuphunzitsa mnzake...Yer 31:34amamwetsa anzake zaukali...Hab 2:15ukonde mnzako ndi kudana...Mat 5:43nanga mnzangayo ndani...Luk 10:29uzikonda mnzako monga...Aro 13:9

MNZANGA (companion)ndiponso iwe, mnzanga weniweni...Afil 4:3ndipo ngati mnzanu wokhulupirika...Chiv 1:9[onaninso: bwenzi]

MOCHENJERA (crafty)apangana mochenjera...Mas 83:3[onaninso: wochenjera]

MOCHENJERERA (deceitfully)osayendayenda mochenjerera...2 Akor 4:2[onaninso: monyenga]

MODEKAI (Mordecai)womuyang’anira Estere; anampatsa uphungu...Est 2:5-20anaulura chiwembu chofuna kupha mfumu...Est 2:21-23anakana kulambira Hamani...Est 3:1-6anapatsidwa ulemu ndi mfumu...Est 6:1-12anakwezedwa kwambiri...Est 8:15; 9:4anakhazikitsa madyerero a Purimu...Est 9:20-31

MODYERA (manger)idzakhala ku chodyetseramo...Yob 39:9namgoneka modyera ng’ombe...Luk 2:7mwana wakhanda atagona modyera...Luk 2:16

MOLEKI (Molech)mulungu wa Aamoni; wopembedzedwa ndi Solomoni...1 Maf11:7anthu anali kuperekedwa nsembe kwa ameneyu...Lev 18:21; 2Maf 23:10

MOLIMBIKA (boldly)m’kunditsegulira mkamwa molimbika...Aef 6:19Potero tilimbike mtima...Aheb 4:16tinena molimbika mtima...Aheb 13:6

MONYENGA (deceitfully)ndipo salumbira monyenga...Mas 24:4[onaninso: mochenjerera]

MOOLOWA MANJA (generously)iye wakufetsa moolowa manja...2 Akor 9:6

MORIYA (Moriah)Mulungu analamula Abrahamu kuti akampereke nsembe Isakipamenepa...Gen 22:1-13malo a kachisi cha Solomoni...2 Mbir 3:1

MOSE (Moses)anabadwa; anabisidwa ndi mai ake; adatengedwa ndi mwana

wamkazi wa Farao...Eks 2:1-10anapha Mwejipito ndi kuthawira ku Midiani...Eks 2:11-22analandira maitanidwe kuchokera kwa Mulungu...Eks 3:1-4:17anabwerera kwa Aisraeli ku Ejipito...Eks 4:18-31anapambana chiombolo cha Aisraeli ndi miliri...Eks

5:1-6:13;6:28-11:10;12:29-42anatsogolera Aisraeli kutuluka mu Ejipito kudzera ku NyanjaYofiira...Eks 13:17-14:31nyimbo yake ya matamando...Eks 15:1-8amapereka kwa anthu zofuna zao modabwitsa...Eks 15:22-17:7anasankha oweruza...Eks 18analandira chilamulo paphiri la Sinai...Eks 19-23analandira malangizo a chihema...Eks 25-31anapembedzera tchimo la Aisraeli...Eks 32anatumidwa ndi kulimbikitsidwa...Eks 33;34malangizo enanso ndi kumanga kwa hema...Eks 35-40anadzodza Aroni...Lev 8:1-36anatenga chiwerengero cha anthu...Num 1:1-54anayamba ulendo wopita ku Kenani...Num 10:11-36anadandaula; akulu ampingo 70 anasankhidwa...Num 11:1-35anapembedzera anthu pamene anakana kulowam’Kenani...Num 14:11-25anagwetsa kuukira kwa Kora...Num 16anachimwa poopsa mtima...Num 20:1-13anapanga njoka ya mkuwa...Num 21:4-9anayenda molunjika Kenani...Num 21:10-20anapanga chiwerengero cha anthu kachiwiri...Num 26asankha Yoswa kukhala wolowa m’malo mwake...Num27:12-23analandiranso malamulo ena...Num 28-30analamula kugonjetsa Midiyani...Num 31malangizo otsiriza...Num 32-36analetsedwa kulowa dziko la malonjezano...Deut 3:23-28anapereka mauthenga a kulawirana...Deut 32,33anaona dziko la malonjezano; anafa...Deut 34:1-7analiridwa ndi kulemekezedwa...Deut 34:8-12anaonekera pamodzi ndi Eliya ndi Khristu pakusandulika...Mat17:1-3

MOTO (fire)Chauta adzagwetsa moto...Gen 19:24ngati malawi a moto...Eks 3:2mumtambo munkayaka moto...Eks 40:38Mulungu amene ayankhe potumiza moto...1 Maf 18:24chivomerezi chija, padafika moto...1 Maf 19:12mtima wanga udangoyaka moto...Mas 39:3tidalowa m’moto ndiponso...Mas 66:12moto umapita patsogolo pake...Mas 97:3inu moto ndi matalala, inu...Mas 148:8kwa anthuwo kumayaka moto...Yes 9:18pamene ukudutsa pamoto...Yes 43:2uli ngati moto wosazima...Yes 65:5naona kuti moto sunathe kutentha...Dan 3:27ndipo motowo udzapsereza...Amo 5:6Chauta ankaitana malawi a moto...Amo 7:4pakuti adzakhala ngati moto...Malak 3:2Mzimu Woyera ndiponso moto...Mat 3:11moto wakenso wowatentha...Marko 9:44ndinabwera kudzaponya moto...Luk 12:49adaona ngati timalawi tamoto...Mac 2:3adzabwera ndi moto woyaka...2 Ates. 1:8lija linali loyaka moto...Aheb 12:18lilime limatentha ngati moto...Yak 3:6pakuwalanga ndi moto wosatha...Yuda 7koma moto udatsika kuchokera...Chiv 20:9zidaponyedwa m’nyanja ya moto...Chiv 20:14

MOTO (oven)ndi mawa oponyedwa pamoto...Mat 6:30

Page 101: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: ng’anjo]

MOWABU (Moab)mwana wa Loti...Gen 19:33-37— Dziko la Amowabu...Deut 1:5

MOYO (life)nauzira mpweya wa moyo...Gen 2:7ndiponso mtengo wa moyo pakati pa...Gen 2:9uzipereka moyo ku moyo...Eks 21:23moyo wa nyama ukhala m’mwazi...Lev 17:11pamaso panu lero lino moyo ndi zokoma...Deut 30:15mwandipatsa moyo ndi...Yob 10:12muli mpweya wa za moyo...Yob 12:10pomchotsera moyo wake...Yob 27:8kuti kuunika kwa moyo...Yob 33:30adzaombola moyo wao kuchinyengo...Mas 72:14mau anu amandipatsa moyo...Mas 119:50safika ku njira za moyo...Miy 2:19mtengo wa moyo wa kuigwira...Miy 3:18wondipeza ine apeza moyo...Miy 8:35anzeru ayenda njira ya moyo...Miy 15:24woyenda ndi mbala ada moyo...Miy 29:24nzeru isunga moyo wa eni ake...Mlal 7:12ndapindapinda moyo wanga...Yes 38:12ndaika pamaso panu njira ya moyo...Yer 21:8udzakhala nao moyo wako ngati...Yer 39:18musadere nkhawa moyo wanu...Mat 6:25moyo wake wa munthu sulingana...Luk 12:15pakuti moyo uli oposa chakudya...Luk 12:23mwa iye munali moyo...Yoh 5:21monga atate ali ndi moyo...Yoh 5:26wopatsa moyo ndi mzimu...Yoh 6:63adzakhala nako kuunika kwa moyo...Yoh 8:12nditaya moyo wanga chifukwa...Yoh 10:15ine ndine kuuka ndi moyo...Yoh 11:25moyo wako kodi udzautaya...Yoh 13:38amene apatsa akufa moyo...Aro 4:17koposa kotani nanga zinthu za moyo...1 Akor 6:3kuti moyonso wa Yesu uoneke...2 Akor 4:10ndili ndi moyo osatinso ine ai... Agal 2:20wozipatsa zinthu zonse za moyo...1 Tim 6:13moyo wanu uli wotani...Yak 4:14adatipatsa ife zonse za pa moyo...2 Pet 1:3ndipo moyowo unaonekera...1 Yoh 1:2matamandidwe a moyo...1 Yoh 2:16Mulungu anatipatsa ife moyo wosatha...1 Yoh 5:11wakukhala ndi mwana ali nawo moyo...1 Yoh 5:12iwo okha olembedwa m’buku la moyo...Chiv 21:27nao ulamuliro pa mtengo wa moyo...Chiv 22:14atenge madzi a moyo...Chiv 22:17gawo lake pa mtengo wa moyo...Chiv 22:19

MOYO (lives)anthu amene anapereka moyo wao...Mac 15:26koma Khristu ali ndi moyo mwa ine...Agal 2:20ife tiyenera kupereka moyo wathu chifukwa cha abale...1 Yoh

3:16ndipo taona ndili wamoyo...Chiv 1:18[onaninso: khala ndi moyo]

MPANDA (hedge)ndipo ndidzammangira mpanda...Hos 2:6koposa mpanda wa minga...Mik 7:4namanga mpanda kuzinga...Marko 12:1[onaninso: tchinga]

MPANDO WA MAPAZI (footstool)khala pansi pa mpando wa mapazi anga...Yak 2:3onaninso: chopondapo mapazi]

MPATA (opportunity)

uchimo udapeza mpata...Aro 7:8nthawi zonse tipeza mpata...Agal 6:10mumkasowa mpata...Afil 4:10

MPHALA (dross)oipa onse apadziko lapansi ngati mphala...Mas 119:119chotsera siliva mphala yake...Miy 25:4kukusiyanitsa ndi mphala yako...Yes 1:25ya Israeli yandikhalira mphala...Ezek 22:18

MPHAMBA (eagle)m’mene imaulukira mphamba...Miy 30:19miphamba imasonkhana kumeneko...Mat 24:28[onaninso: chiwombankhanga, mphungu]

MPHAMVU (ability)achite ngati mumphamvu...1 Pet 4:11[onaninso: kukhoza, kutha, nzeru]

MPHAMVU (abundance)analemera ndi mphamvu ya kudyerera kwake...Chiv 18:3[onaninso: chuluka, chuma, ukulu, sefukira,yambiri, zonona]

MPHAMVU (authority)mphamvu zonse zapatsidwa kwa Ine...Mat 28:18adapatsa mwanayu mphamvu...Yoh 5:27pajatu mudapatsidwa mphamvu...Yoh 17:2adakhazikitsa mwa mphamvu yawo...Mac 1:7[onaninso: olamulira, ulamuliro]

MPHAMVU (force)aukwatula ndi mphamvu...Mat 11:12mphamvu atafa mwini wake...Aheb 9:17

MPHAMVU (might)mphamvu za ntchito...Mas 145:6mphamvu zake zazikulu...Yes 40 :26asadzitamandire mphamvu...Yer 9:23mphamvu yao yalephereka...Yer 51:30nkhondo ai ndi mphamvu ai...Zek 4:6mkulimbana kwa mphamvu...Aef 6:10polimbitsa mphamvu...2 Pet 2:11ndi mphamvu zikhale kwa...Chiv 7:12

MPHAMVU (mighty)ndiye mpalu wamphamvu...Gen 10:9popeza andiposa mphamvu...Num 22:6Ha! adagwa amphamvu...2 Sam 1:19ndi wamphamvu yaikulu...Yob 9:4

MPHAMVU (power)muwone mphamvu zanga...Eks 9:16ndi mphamvu ku nkhondoko...2 Mbir 25:8kukula kwa mphamvu...Yob 26:14mphamvu ndi zanu...Mas 62:11mphamvu zanu nzazikulu...Mas 66:3ndiye amapatsa mphamvu...Mas 68:35munthu alibe mphamvu...Mlal 8:8wandidzadza ndi mphamvu...Mika 3:8chauta ndi wamphamvu zedi...Nah 1:3nkhondo kapena mphamvu...Zek 4:6pakuti ufumu, mphamvu...Mat 6:13munthu ali nazo mphamvu...Mat 9:6ngakhalenso mphamvu za...Mat 22:29mphamvu zochokera kwa...Luk 5:17mphamvu zinkatuluka mwa iye...Luk 6:19mpaka mutalandira mphamvu...Luk 24:49ndili nazo mphamvu...Yoh 10:18ine ndili ndi mphamvu...Yoh 19:10akadapanda kukupatsani mphamvu...Yoh 19:11koma mudzalandira mphamvu...Mac 1:8ndi mphamvu zathu zathu...Mac 3:12

Page 102: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndiye mphamvu ya Mulungu...Mac 8:10mutandipatsako inenso mphamvu...Mac 8:19ndi mphamvu ya Mulungu...Aro 1:16mphamvu zake nzosatha...Aro 1:20mauwo ndi mphamvu...1 Akor 1:18Khristu ndi mphamvu ya...1 Akor 1:24mphamvu zanga zimaoneka...2 Akor 12:9mphamvu yake yopirira...Aef 1:19adaonetsapo mphamvu...Aef 3:7Ambuye mwa mphamvu yao...Aef 6:10mphamvu yake yaulemerero...Akol 1:11ulemerero wa mphamvu...2 Ates 1:9Mzimu wotipatsa mphamvu...2 Tim 1:7ndi mau ake amphamvu...Aheb 1:3anali ndi mphamvu...Aheb 2:14chifukwa cha mphamvu...Aheb 7:16Mulungu mwa mphamvu...2 Pet 1:3ulemerero, ukulu, mphamvu...Yuda 25ulemerero, ulemu ndi mphamvu...Chiv 4:11[onaninso: nyonga]

MPHAMVU (powerful)Chauta ndi la mphamvu...Mas 29:4ogwira ntchito mwamphamvu...Aheb 4:12

MPHAMVU (powers)ndi mphamvu za nthawi...Aheb 6:5[onaninso: maulamuliro]

MPHANDA (boughs)unatambalitsa mphanda zake...Mas 80:11[onaninso: nthambi]

MPHANDA (branch)ku mphanda ina...Eks 25:33[onaninso: nthambi]

MPHASA (bed)unayala mphasa yako...Yes 57:7[onaninso: kama, pogona, tchika]

MPHATSO (gift)mphatso ya munthu imakhala...Miy 18:16mphatso ya mtseri ipembedza mkwiyo...Miy 21:14ndi mphatso ya Mulungu kwa anthu...Mlal 3:13mukadadziwa mphatso ya Mulungu...Yoh 4:10mphatso yaulere ya Mulungu...Aro 5:15mphatso yaulere ya Mulungu amapereka...Aro 6:23Mulungu adapatsa munthu aliyense mphatso...1 Akor 7:7ngakhale nditakhala ndi mphatso ya uneneri...1 Akor 13:2kupulumuka kwanu ndi mphatso ya Mulungu...Aef 2:8sikuti ndikuika mtima pa mphatso zanu...Afil 4:17usanyozere mphatso yaulere ija ili mwa iwe...1 Tim 4:14mphatso imene Mulungu adakupatsa...2 Tim 1:6mphatso yochokera kumwamba...Aheb 6:4mphatso iliyonse yabwino ndi yangwiro...Yak 1:17mphatso imene adalandira kwa Mulungu...1 Pet 4:10

MPHATSO (gifts)mphatso zonse zimene mwalandira...Num 18:29mudalandira mphatso kwa anthu...Mas 68:18Seba adzabwera ndi mphatso...Mas 72:10ngakhale umpatse mphatso zochuluka...Miy 6:35mumadziwa kupatsa ana anu mphatso...Mat 7:11tili ndi mphatso zosiyanasiyana...Aro 12:6pali mphatso zamitundumitundu...1 Akor 12:6mphatso zimene Mzimu Woyera amapereka...1 Akor 14:1adagawira anthu mphatso...Aef 4:8[onaninso: zopereka]

MPHAWI (poor)amphawi amawalimbitsa mtima...Yob 5:16

adapondereza amphawi...Yob 20:19ndinkapulumutsa amphawi olira...Yob 29:12munthu wa umphawi...Miy 10:4m’mphawi ngakhale anzake...Miy 14:20amachitira chifundo amphawi...Miy 14:21wopondereza m’mphawi...Miy 14:31amene amalalatira mphawi...Miy 17:5m’mphawi usamubere...Miy 22:22alendo ndiponso amphawi...Zek 7:10amphawi akumva uthenga wabwino...Mat 11:5adakhala m’mphawi...2 Akor 8:9anthu ao aumphawi...Agal 2:10ooneka amphawi m’maso...Yak 2:5mukunyoza mphawiyo...Yak 2:6ochititsa chifundo, amphawi...Chiv 3:17[onaninso: osauka, wosauka]

MPHEKETSERA (rumour)padzakhala mpheketsera...Ezek 7:26ndi mpheketsera za nkhondo...Mat 24:6kapena mpheketsera za nkhondo...Marko 13:7

MPHEPO (wind)mphepo yamphamvu idaomba...1 Maf 19:11mphepo yakuvuma imamuulutsa...Yob 27:21mungu wouluzika ndi mphepo...Mas 1:4akaombetsa mphepo, madzi...Mas 147:18mphepo ikhale bwino...Mlal 11:4sudziwa njira ya mphepo...Mlal 11:5iwe mphepo yakumpoto...Nyi 4:16azingopita ngati mphepo...Yer 5:13amakunthitsa mphepo...Yer 51:16amanka nasaka mphepo...Hos 12:1mapiri ndi kupanga mphepo...Amo 4:13bango logwedezeka ndi mphepo...Mat 11:7ndipo adadzudzula mphepoyo...Marko 4:39adadzuka, naletsa mphepoyo...Luk 8:24mphepo imaombera kumene...Yoh 3:8nkokomo ngati wa mphepo...Mac 2:2otengekatengeka ndi mphepo...Aef 4:14

MPHEPO (winds)kuchokera ku mphepo zinai...Ezek 37:9kuti ngakhale mphepo ndi nyanja...Mat 8:27akugwira mphepo zinai...Chiv 7:1

MPHESA (grapes)chake m’mwazi wa mphesa...Gen 49:11mphesa zao ndizo mphesa za ndulu...Deut 32:32unangobala mphesa zosadya...Yes 5:2sipadzakhala mphesa pa mpesa...Yer 8:13wakuti atate adadya mphesa...Ezek 18:2kodi atchera mphesa pa minga...Mat 7:16pakuti mphesa zake zapsa...Chiv 14:18[onaninso: mipesa]

MPHEZI (lightning)mphezi zake zinaunikira...Mas 97:4pakuti monga mphezi idzera...Mat 24:27kuonekera kwake kunali ngati mphezi...Mat 28:3satana alimkugwa ngati mphezi...Luk 10:18panali mabingu ndi mphezi...Eks 19:16mphezi zanu zinawalitsa...Mas 77:18wachifumu munatuluka mphezi...Chiv 4:5

MPHINDI (moment)kuti ndiwathe mkamphindi...Num 16:21mkamphindi akufa...Yob 34:20nkhope yanga mkamphindi...Yes 54:8mkamphindi mkutama...1 Akor 15:52[onaninso: kanthawi]

Page 103: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

MPHIRI (cobra)chidzakhala ndulu ya mphiri...Yob 20:14akunga mphiri yogontha mkhutu...Mas 58:4udzaponda mkango ndi mphiri...Mas 91:13dzanja lake pafunkha la mphiri...Yes 11:8

MPHONJE (hem)nakhudza mphonje ya chofunda...Mat 9:20akhudze yokha mphonje ya...Mat 14:36

MPHOTHO (prize)ndiye amalandira mphotho...1 Akor 9:24kuti ndikalandire mphotho...Afil 3:14

MPHOTHO (reward)mphotho yako idzakhala yayikulu...Gen 15:1ndimalandira mphotho yayikulu...Mas 19:11olungama amalandiradi mphotho...Mas 58:11amalandira mphotho yeniyeni...Miy 11:18Chauta adzakupatsa mphotho...Miy 25:22mphotho ya ntchito zanga...Mlal 2:10watsogoza mphotho...Yes 40:10mphotho yanu ndiyaikulu...Mat 5:12simudzalandira mphotho kwa Atate...Mat 6:1amenewa alandiriratu mphotho...Mat 6:2adalandira mphotho ya nthumwi...Mat 10:41sadzalephera kulandira mphotho...Mat 10:42mudzalandira mphotho yaikulu...Luk 6:35aliyense adzalandira mphotho yake...1 Akor 3:8asakuletseni kupata mphothoyo...Akol 2:18anali ndithu pa mphotho...Aheb 11:26kuti mukalandire mphotho...2 Yoh 8ndikubwera ndi mphotho yanga...Chiv 22:12[onaninso: bwezera, landira]

MPHUMI (foreheads)ukaike chizindikiro pamphumi...Ezek 9:4chizindikiro cha Mulungu chija pamphumi...Chiv 9:4chizindikiro chija pa mphumi...Chiv 20:4

MPHUNGU (eagle)ngati mphungu imene ikuphunzitsa...Deut 32:11ngati mphungu yogudukira...Yob 9:26athamanga kopambana mphungu...Yer 4:13monga m’mene mphungu...Eks 19:4[onaninso: chiwombankhanga, mphamba]

MPHUNO (nostrils)wopatsa moyo mphuno...Gen 2:7wa Mulungu mphuno...Yob 27:3wake uli m’mphuno...Yes 2:22

MPHUTHU (doorposts)alembeni pa mphuthu za zitseko...Deut 6:9[onaninso: mitu ya nsanamila]

MPIKISANO WA LIWIRO (race)monga inu simudziwa kuti pa mpikisano wa liwiro...1 Akor9:24ndatsiriza bwino mpikisano wa liwiro...2 Tim... 4:7[onaninso: kuthamanga]

MPINGO (church)ndidzamanga mpingo...Mat 16:18ukauze mpingo...Mat 18:17akuru mosankha mu mpingo...Mac 14:23mufuna kunyazitsa mpingo...1 Akor 11:22kuti kudzera mwa mpingo...Aef 3:10Khristu adakondera mpingo...Aef 5:25monga momwe Khristu amachitira mpingo...Aef 5:29

thupi lake, ndiye kuti mpingo...Akol 1:24osasenzetsa mpingo katundu...1 Tim 5:16

MPULUMUTSI (deliverer)mpulumutsi amene anawapulumutsa...Ower 3:9Yehova Israeli mpulumutsi...2 Maf 13:5adzatuluka ku Ziyoni mpulumutsi...Aro 11:26

MPULUMUTSI (saviour)Mulungu mpulumutsi wao...Mas 106:21iye adzatuma mpulumutsi...Yes 19:20wa Israeli, mpulumutsi wako...Yes 43:3Mulungu wolungama ndi Mpulumutsi...Yes 45:21Chauta ndine mpulumutsi...Yes 60:16Iye anali Mpulumutsi wao...Yes 63:8mpulumutsi wako ndine...Hos 13:4Mulungu mpulumutsi wanga...Luk 1:47wakubadwirani mpulumutsi...Luk 2:11ameneyu ndi mpulumutsi...Yoh 4:42Mtsogoleri ndi Mpulumutsi...Mac 5:31kuti akhale mpulumutsi...Mac 13:23Iye mwini ndi mpulumutsi...Aef 5:23Mulungu, mpulumutsi wathu...1 Tim 1:1amene ali mpulumutsi...1 Tim 4:10m’kuwoneka kwa mpulumutsi...2 Tim 1:10Mpulumutsi wathu Yesu...Tit 2:13[onaninso: pulumutsa]

MPWEYA (breath)nauzira mpweya wa moyo...Gen 2:7mpumo wa mpweya...2 Sam 22:16atayika ndi mpweya wa Mulungu...Yob 4:9ndi mpweya wa Mulungu...Yob 27:3ndi mpweya wamphamvu...Yob 33:4mukalanda mpweya wao...Mas 104:29munthu akunga mpweya...Mas 144:4onse ali ndi mpweya umodzi...Mlal 3:19amapatsa anthu am’menemo mpweya...Yes 42:5ndidzalonga mpweya mwa inu...Ezek 37:5m’dzanja mwake muli mpweya wanu...Dan 5:23apatsa zonse moyo ndi mpweya...Mac 17:25fano la chirombo mpweya...Chiv 13:15[onaninso: puma]

MSAMARIYA (samaritan)koma Msamariya wina ali...Luk 10:33mai wachisamariya...Yoh 4:9

MSAMPHA (snare)mudzakodwa mu msampha...Eks 23:33ndipo idasanduka msampha...Ower 8:27ngati msampha kwa Davideyo...1 Sam 18:21msampha wamkola...Yob 18:8zao zisanduke msampha...Mas 69:22ngati mbalame mu msampha...Mas 124:7zimakodwera mu msampha...Mlal 9:12ndi zenje ndi msampha zili pa iwe...Yes 24:17ndakutchera iwe msampha...Yer 50:24mneneriyo amtchera msampha...Hos 9:8nkukatera pa msampha...Amo 3:5lidzawagwera ngati msampha...Luk 21:35amagwidwa mu msampha...1 Tim 6:9adzapulumuka mu msampha ...2 Tim 2:26[onaninso: dzenje]

MSANA (back)koma wopusa pamsana pake nthyole...Miy 10:13ntyole iyenera pamsana pa zitsiru...Miy 26:3ndinapereka msana wanga kwa omenya...Yes 50:6[onaninso: m’mbuyo]

MSASA (tent)nyumba ya pansi pano ya msasa wathu...2 Akor 5:1

Page 104: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

pokhala ine msasa uwu...2 Pet 1:13kuleka kwa msasa wanga kuli pafupi...2 Pet 1:14[onaninso: hema]

MSEU (road)ndikulambula mseu mchipululu...Yes 43:19[onaninso: njira]

MSILIKALI (soldier)zowawa monga msilikali...2 Tim 2:3msilikali amene akumenya...2 Tim 2:3

MSINKHU (age)ali wa msinkhu...Yoh 9:21[onaninso: kalamba, zaka]

MSIRIRO (covetousness)mundisungire kupewa msiriro...Luk 12:15[onaninso: chisiriro, sirira, kangamira]

MSONKHANO (assembly)kudzapha msonkhano...Eks 16:3muzichita msonkhano...Lev 23:36dzina lanu pamsonkhano…Mas 22:22ndidana nawo msonkhano wa anthu ochimwa...Mas 26:5mu msonkhano wa oyera mtima...Mas 89:5mu msonkhano wa anthu...Mas 89:7msonkhano wa akufa...Miy 21:16itanitsani msonkhano wa ulemu...Yow 1:14sonkhanitsani anthu pamodzi...Yow 2:16ndidzakutamandani pamsonkhano wa anthu...Aheb 2:12kumene kwasonkhana ana oyamba ...Aheb 12:23

MSONKHANO (congregation)mu msonkhano wa olungama...Mas 1:5msonkhano wa oipa wandisokoneza...Mas 22:16aima mu msonkhano wa Mulungu...Mas 82:1

MTAMBO (cloud)utawaleza wa mtambo...Gen 9:13unawatsogolera usana ndi mtambo...Eks 13:21ndi mtambo unaphimba phiriro...Eks 24:15mtambo uja udatsika...Eks 33:9mtambo woti njo sunawachokera...Neh 9:19msana unawatsogolera ndi mtambo...Mas 78:14kukoma mtima kwake kunga mtambo...Miy 16:15amene auluka ngati mtambo...Yes 60:8kukoma mtima kwako kukunga mtambo...Hos 6:4mtambo wowala unawaphimba...Mat 17:5mwana wa munthu alimkudza mu mtambo...Luk 21:27ndipo mtambo unamlandira Iye...Mac 1:9makolo athu onse anali pansi pa mtambo...1 Akor 10:1tizingidwa nao mtambo waukuru...Aheb 12:1

MTANDA (cross)amene sasenza mtanda wake...Mat 10:38kuti anyamule mtanda wake...Mat 27:32tatsika pamtandapo...Mat 27:40mtanda wa Khristu ungayesedwe...1 Akor 1:17ungazunzike chifukwa cha mtanda...Agal 6:12koma mu mtanda wa Ambuye...Agal 6:14limodzi mwa mtandawo ...Aef 2:16ali adani a mtanda wa Khristu...Afil 3:18anapirira mtanda...Aheb 12:2

MTANGA (basket)zidzakhala zotembereredwa mtanga mwanu...Deut 28:17mtanga umodzi unali ndi nkhuyu...Yer 24:2mumtanga ananditsitsa...2 Akor 11:33[onaninso: mbiya]

MTEMBO (body)

napempha mtembo wake...Mat 27:58[onaninso: thupi]

MTEMBO (carcass)iye kukaona mtembo wa mkango...Owe 14:8kumene kulikonse kuli mtembo...Mat 24:28

MTEMBO (coffin)mtembo wake adaukonza ndi mankhwala...Gen 50:26[onaninso: chithatha]

MTEMBO (corpse)mtembo wake unagwera m’njiramo...1 Maf 13:24monga ngati mtembo wopondedwa...Yes 14:19

MTENDERE (ease)ndidaali pa mtendere...Yob 16:12[onaninso: kukhala mosavuta, pumula]

MTENDERE (peace)anthu amenewa ali a mtendere...Gen 34:21ndipo ndidzapatsa mtendere...Lev 26:6pa iwe, nakupatse mtendere...Num 6:26mupangane nane za mtendere...2 Maf 18:31zidzakhala nawe mu mtendere...Yob 5:23ndi mtendere ndidzagona pansi...Mas 4:8funa mtendere ndi kuulondola...Mas 34:14adzalankhula za mtendere...Mas 85:8ali nao mtendere wambiri...Mas 119:165ine ndikuti mtendere...Mas 120:7mupempherere mtendere wa...Mas 122:6mwako mukhale mtendere...Mas 122:7mtendere ukhale pa Israeli...Mas 125:5ndi mphindi ya mtendere...Mlal 3:8kalonga wa mtendere...Yes 9:6wokhazikika mu mtendere weniweni...Yes 26:3njira ya mtendere saidziwa...Yes 59:8kuti, mtendere, mtendere...Yer 6:14tinayang’anira mtendere...Yer 8:15ndidzakupatsani mtendere weniweni...Yer 14:13adzafunafuna mtendere...Ezek 7:25dziko lonse lapansi, mtendere...Dan 4:1ameneyo adzakhala mtendere...Mik 5:5muno ndidzapatsa mtendere...Hag 2:9anthu odzetsa mtendere...Mat 5:9mtendere wanu udze pa...Mat 10:13Ndidadzera kuponya mtendere...Mat 10:34mtendere pansi pano mwa...Luk 2:14mukakhala mwana wa mtendere...Luk 10:6iwetu zinthu za mtendere...Luk 19:42ndikukupatsani mtendere wanga...Yoh 14:27kuti mukhale nao mtendere...Yoh 16:33ndikukupatsani mtendere...Aro 1:7khalani ndi mtendere ndi anthu...Aro 12:18tili pa mtendere ndi Mulungu...Aro 5:1mukhale ndi moyo wa mtendere...1 Akor 7:15wachikondi ndi wa mtendere...2 Akor 13:11chikondi, chimwemwe, mtendere...Agal 5:22ndiye mtendere wathu...Aef 2:44mtendere wochokera kwa Mulungu...Afil 4:7zimenezi pakudzetsa mtendere...Akol 1:20mtendere wa Khristu...Akol 3:15muzikhalitsana ndi mtendere...1 Ates 5:13chikhulupiriro, chikondi ndi mtendere...2 Tim 2:22“Mfumu ya mtendere...Aheb 7:2amafetsa mu mtendere...Yak 3:18kukupatsani mtendere wochuluka...2 Pet 1:2wa bata ndi wa mtendere...1 Tim 2:2kuwonjeza apo za mtendere...Yak 3:17

MTENGO WAPATALI (precious)ngati wa mtengo wapatali...1 Sam 26:21

Page 105: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi ya mtengo wapatali pamaso...Mas 116:15zolingalira zanu za mtengo wache...Mas 139:17yoposa miyala ya mtengo wapatali...Miy. 3:15ndiwe wamtengo wapatali pamaso...Yes 43:4ukasiyanitsa cha mtengo wache...Yer 15:19ana a Ziyoni a mtengo wapatali...Mali 4:2ndiwo a mtengo wache woposa...1 Pet 1:7iye ndi wamtengo wapatali...1 Pet 2:7moyo wotere ngwamtengo wapatali...1 Pet 3:4

MTENGO (plant)ngati mtengo wa mpesa...Yer 144:12[onaninso: bzyala]

MTENGO (cost)nawerengera mtengo wake...Luk 14:28

MTENGO (price)mtengo wake sangayerekeze...Yob 28:15kodi bwanji mtengo wogulira...Miy 17:16imodzi ya mtengo wapatali...Mat 13:46ndi kupatula pa mtengo wake...Mac 5:3adakugulani ndi mtengo...1 Akor 6:20

MTHANDIZI (help)koma panalibe mthandizi...Mas 107:12Yehova, ndiye mthandizi wao...Mas 115:9[onaninso: thandiza, thandizo]

MTHANDIZI (helper)Mulungu ndiye mthandizi wanga...Mas 54:4mthandizi wanga ndiye Ambuye...Aheb 13:6[onaninso: nkhoswe]

MTHENGA (angel)mthenga wa Yehova anaturuka...2 Maf 19:35[onaninso: mngelo]

MTHENGA (messanger)mthenga wokhulupirika ...Miy 25:13ndituma mthenga...Mal 3:1ndituma mthenga...Mat 11:10

MTHUNZI (shade)pakukhala pa mthunzi wake...Nyi 2:3padzakhala chihema cha mthunzi...Yes 4:6kubindikira mumthunzi wake...Marko 4:32

MTHUNZI (shadow)mdimandi mthunzi wa imfa...Job 3:5amathawa ngati mthunzi...Job 14:2ndifungatireni mu mthunzi wanu...Mas 17:8munthu ayenda ngati mthunzi...Mas 39:6ali ngati mthunzi...Mas 144:4autsiriza ngati mthunzi...Mlal 6:12ndi kukhulupirira mthunzi wa...Yes 30:2mu mthunzi wa dzanja lake wandibisa...Yes 49:2ndizo mthunzi wa zirinkudzazo...Akol 2:17pokhala nao mthunzi wa zokoma...Aheb 10:1kapena mthunzi wa chitembenukiro...Yak 1:17

MTIMA UMODZI (accord)ndi mtima umodzi...Yos 9:2kumtumikira ndi mtima umodzi...Zef 3:9kupemphera ndi mtima umodzi...Mac 1:14ndi mtima umodzi mkachisi...Mac 2:46olingalira mtima umodzi...Afil 2:2

MTIMA (heart)pakuti mudziwa mtima wa mlendo...Eks 23:9kunali zotsimikiza mtima zazikulu...Owe 5:16mtima wanga umyuka mokondwera...1 Sam 2:1

anampatsa mtima wina watsopano...1 Sam 10:9koma Yehova ayang’ana mumtima...1 Sam 16:7akazi ake anapambutsa mtima wake...1 Maf 11:4Mulungu walefula mtima wanga...Yob 23:16ukhale moyo mtima wako...Mas 22:26mtima wanga usefukira nacho...Mas 45:1mtima wanga wakhazikika...Mas 57:7pakuti mtima wanga udawawa...Mas 73:21mtima wanga ndi thupi langa...Mas 84:2mtima wopulukira udzandichokera...Mas 101:4wodzikuza ndi mtima wodzitama...Mas 101:5ndidzayamika Yehova ndi mtima wonse...Mas 111:1mtima wanga sunadzikuza...Mas 131:1mtima wokondwa usekeretsa nkhope...Miy 15:13mtima wa mfumu uli m’dzanja la Yehova...Miy 21:1koma mtima wake suli pa iwe...Miy 23:7yofunitsitsa ndi mtima woipa...Miy 26:23wokhulupirira mtima wake wake...Miy 28:26mtima wa anzeru uli m’nyumba ya...Mlal 7:4ndipo mtima wa munthu wanzeru...Mlal 8:5mtima wanga ndi kuguguda...Nyi 5:4ndi mtima wonse walefuka...Yes 1:5ndi za m’mtima mwanga zilirira...Yes 16:11zofunafuna za mtima wanu ndi chisoni...Yes 63:15amene ayesa imso ndi mtima...Yer 11:20mtima ndiwo wonyenga koposa...Yer 17:9pakuti adzabwera kwa ine ndi mtima wao...Yer 24:7chifukwa chake mumtima mwanga ndimlira...Yer 31:20ndidzawapatsa mtima umodzi...Ezek 11:19ndi kudzifunira mtima watsopano...Ezek 18:31achilendo osadulidwa mtima...Ezek 44:7komweko udzakhale mtima...Mat 6:21pakuti mu mtima muchokera...Mat 15:19mtima wake udzakhala ngati...Yoh 7:38mtima wanu usavutike...Yoh 14:1linali la mtima umodzi...Mac 4:32walola mtima wako kugwidwa ndi...Mac 5:3pakuti mtima wako suli wolungama...Mac 8:21ndipo ukhulupirira mu mtima mwako...Aro 10:9muzichita zimenezi ndi mtima woona...Aef 6:5utsitsimutse mtima wanga mwa...Fil 20iye nkumuumira mtima namumana...1 Yoh 3:17pamene mtima wathu ukutitsutsa...1 Yoh 3:20[onaninso: mitima]

MTIMA (heartily)muchichite ndi mtima wonse...Akol 3:23

MTOVU (lead)m’madzi akulu ngati mtovu...Eks 15:10[onaninso: tsogolera]

MTSERI (corner)ichi sichinachitika mtseri...Mac 26:26

MTSERI (secret)ntchito ya manja a mmisiri ndi kuliika m’malo a mtseri...Deut27:15mphatso ya mtseri ipembedza mkwiyo...Miy 21:14ndi zolemera zobisika za m’malo a mtseri...Yes 45:3kuyambira pachiyambi sindidanene mtseri...Yes 48:16moyo wanga udzalira mtseri chifukwa cha kunyadakwanu...Yer 13:17mphatso zako zachifundo zikhale zamtseri...Mat 6:4Atate wako wakuona mtseri...Mat 6:4nupemphere Atate wako ali mtseri...Mat 6:6ndipo Atate wako akuona mtseri adzakubwezera iwe...Mat 6:6koma kwa Atate wako ali mtseri...Mat 6:18ndipo Atate wako wakuona mtseri adzakubwezera iwe...Mat

6:18palibe kanthu kanakhala ka mtseri...Marko 4:22pakuti chochitidwa nao mtseri...Aef 5:12

Page 106: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: bisalika, bisika, chinsinsi]

MTSINJE (brook)miyala isanu yosalala ya mtsinje...1 Sam 17:40adzamwa ku mtsinje...Mas 110:7kunka ku tsidya lina la mtsinje...Yoh 18:1

MTSINJE (river)madzi a mumtsinje...Yob 40:23madzi a mumtsinje wa madalitso...Mas 36:8mtsinje umene mifuleni...Mas 46:4mtsinje wa Mulungu ndi wodzadza...Mas 65:9anthu adaoloka mtsinje...Mas 66:6mtendere ngati mtsinje...Yes 66:12nkumawabatiza mtsinje...Marko 1:5adandionetsa mtsinje...Chiv 22:1

MTSOGOLERI (prince)akhale Mtsogoleri ndi Mpulumutsi...Mac 5:31[onaninso: kalonga, mkulu]

MTSUKO (pot)Aaroni kuti, “tenga mtsuko...Eks 16:33[onaninso: mbiya, nkhali]

MTUMIKI (ambassador)koma mtumiki wokhulupirika..Miy 13:17ndiri mtumiki...Aef 6:20chifukwa chake tiri atumiki...2 Akor 5:20

MTUMIKI (minister)iwe ukhale mtumiki…Mac 26:16ndiye mtumiki wa Mulungu...Aro 13:4udzakhala mtumiki...1 Tim 4:6mtumiki wa malo opatulika...Ahe 8:2[onaninso: kapolo]

MTUMIKI (servant)osakhala mtumiki...Yes 42:19akhale mtumiki wanga...Mat 20:26ndiwe mtumiki wabwino...Mat 25:21mtumiki wopanda pakeyo...Mat 25:30[onaninso: kapolo]

MTUMWI (apostle)mtumwi woitanidwa...Aro 1:1ndi mtumwi wathu...Aro 11:13kodi sindine mtumwi...1 Akor 9:1zizindikirotu za mtumwi...2 Akor 12:12ine mlaliki wake ndi mtumwi...1 Tim 2:7lingilirani za mtumwi...Aheb 3:1

MTUNDU (nation)ndidzakuyesa mtundu waukulu...Gen 12:2kodi mudzaphanso mtundu...Gen 20:4ansembe ndi mtundu wopatulika...Eks 19:6anthu a mtundu wina...Mas 147:20chilungamo chikuza mtundu...Miy 14:34mtundu sudzanyamula lupanga...Yes 2:4kuti mtundu wolungama...Yes 26:2wochepa adzasanduka mtundu...Yes 60:22kwa mtundu umene sunatchula...Yes 65:1mtundu wa anthu unasintha...Yer 2:11ndidzawayesa mtundu umodzi...Ezek 37:22anthu a mtundu wako...Dan 12:1mtundu umodzi wa anthu...Mat 24:7akonda mtundu wathu...Luk 7:5sakhala mtundu wa anthu...Aro 10:19[onaninso: mitundu]

MUHEBRI (hebrew)liwu lopatsidwa kwa:

Abramu...Gen 14:13Aisraeli...1 Sam 4:6,9Ayuda...Mac 6:1Paulo...Afil 3:5

MULUNGU WACHIKAZI (goddess)ankapembedza Asitoreti, mulungu wachikazi...1 Maf 11:5

MULUNGU (God)Mulungu adalenga kumwamba ndi ...Gen 1:1nati, Abramu adalitsike ndi Mulungu...Gen 14:19ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wao...Gen 17:8Mulungu wa Abrahamu...Eks 3:6ameneyo ndiye Mulungu wanga...Eks 15:2ukhale m’malo mwa anthu kwa Mulungu...Eks 18:19ndine Yehova Mulungu...Eks 20:2Mulungu sindiye munthu...Num 23:19Mulungu wanu ndiye moto...Deut 4:24Mulungu wamkulu ndi woopsa...Deut 7:21Mulungu wanu ndiye Mulungu wanga...Rut 1:16kuti kwa Israeli kuli Mulungu...1 Sam 17:46thanthwe ndani, koma Mulungu wathu...2 Sam 22:32ngati Yehova ndiye Mulungu...1 Maf 18:21Mulungu wathu ndiye wamkulu...Yob 33:12Mulungu ndiye mwini mphamvu...Yob 36:5Mulungu ndiye wamkulu...Yob 36:26Mulungu wanga ndinu....Mas 22:10Mulungu wako ali kuti...Mas 42:3Mulungu ndiye pothawirapo pathu...Mas 46:1Mulungu ali mkati mwake...Mas 46:5Mulungu ndiye mfumu ya dziko lonse...Mas 47:7Mulungu wa Mulungu...Mas 50:1Ine Mulungu ndine Mulungu wako...Mas 50:7mtima woyera, Mulungu...Mas 51:10Mulungu akhala kwa ife Mulungu...Mas 68:20Mulungu wamkulu ndani monga Mulungu...Mas 77:13Mulungu wamakamu mutibweze...Mas 80:7Inu ndinu Mulungu nokhanu...Mas 86:10mkwezeni Yehova Mulungu wathu...Mas 99:9Mulungu wathu ngwa nsoni...Mas 116:5yamikani Mulungu wakumwamba...Mas 136:26pakuti Mulungu ali kumwamba...Mlal 5:2wauphungu, Mulungu wamphamvu...Yes 9:6Mulungu ndiye chipulumutso changa...Yes 12:2uyu ndiye Mulungu wathu...Yes 25:9taonani Mulungu wanu...Yes 40:9popanda Ine aliponso Mulungu...Yes 44:8Ziyoni, Mulungu wako ndi mfumu...Yes 52:7wokankhidwa ndi Mulungu...Yes 53:4ndidzakhala Mulungu wao...Yer 31:33ndinaona masomphenya a Mulungu...Ezek 1:1ndani Mulungu wofanana ndi Inu...Mik 7:18ndilo losandulika Mulungu...Mat 1:23mwa Mulungu mpulumutsi wanga...Luk 1:47ndipo mau anali kwa Mulungu...Yoh 1:1sakhoza kulowa ufumu wa Mulungu...Yoh 3:5pakuti Mulungu anakonda dziko...Yoh 3:16chizindikiro chake kuti Mulungu ali...Yoh 3:33Mulungu ndiye mzimu...Yoh 4:24Ambuye wanga ndi Mulungu wanga...Yoh 20:28Mulungu adzatuma wina kuchokera...Mac 7:37Yesu Khristu ndi mwana wa Mulungu...Mac 8:37kwa Mulungu wosadziwika...Mac 17:23zimene Mulungu amalankhula nzoonadi...Aro 3:4ngati Mulungu ali pa mbali yathu...Aro 8:31Mulungu ndi wokhulupirika...1 Akor 1:9kwa ife, Mulungu ndi m’modzi yekha...1 Akor 8:6Mulungu wanga adzakwaniritsa...Afil 4:19ndidzakhala Mulungu wao...Aheb 8:10Mulungu wathu ndi moto wopsereza...Aheb 12:29Mulungu ndi wamkulu kopambana...1 Yoh 3:20Mulungu ndiye chikondi...1 Yoh 4:8

Page 107: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

palibe munthu amene adaona Mulungu...1 Yoh 4:12mnyumba ya Mulungu wanga...Chiv 3:12Mulungu mwini adzakhala nao...Chiv 21:3ndidzakhala Mulungu wake...Chiv 21:7

MUNDA WA MAGAZI (field of blood)munda womwe unagulidwa kukhala manda omuikiramoYudasi...Mat 27:1-10unaloseredwa m’chipangano chakale...Zek 11:12,13

MUNDA WA M’MISIRI (potter’s field)agule munda wa m’misiri...Mat 27:7,8

MUNDA (field)munda ukondwere ndi zonse...Mas 96:12amene aphatikiza munda ndi munda...Yes 5:8chidzasanduka munda wobalitsa...Yes 32:15munda ndiwo dziko lapansi...Mat 13:38nagula munda umenewu...Mat 13:44chifukwa chake munda umenewu...Mat 27:8inuyo ndinu munda wa Mulungu...1 Akor 3:9

MUNDA (garden)Mulungu anadzala m’munda...Gen 2:8mkwatibwi ndiye munda...Nyi 4:12udzafanana ndi munda wothirira madzi...Yes 58:11m’Edeni, munda wa Mulungu...Ezek 28:13kumene kunali munda...Yoh 18:1koma kunali munda kumalo...Yoh 19:41

MUNDA (ground)ndagula munda ndipo...Luk 14:18[onaninso: malo, nthaka]

MUNGU (chaff)ngati mungu wouluzika...Yob 21:8koma akunga mungu wouluka...Mas 1:4akhale monga mungu kumphepo...Mas 35:5mudzatenga pakati ndi mungu...Yes 33:11tsiku lisanapitirire ngati mungu...Zef 2:2[onaninso: mankhusu]

MUNTHU WOLANKHULA NDI MIZIMU (medium)kapena mkazi wolankhula ndi mizimu...Lev 20:27aliko mkazi wolankhula ndi mizimu...1 Sam 28:7

MUNTHU (man)tipange munthu mchifanizo...Gen 1:26munthuyo ndinu nomwe..2 Sam 12:7munthu ndani kuti mumkuze...Yob 7:17munthu wopanda pake asowa...Yob 11:12ndiwe munthu woyamba kubadwa...Yob 15:7munthu ndani kuti mumkumbukire...Mas 8:4adzandichitanji munthu...Mas 118:6kwa mwana wa munthu...Mat 24:27ananena nao, taonani munthuyu...Yoh 19:5monga imfa inadza mwa munthu...1 Akor 15:21koma ungakhale umunthu wathu...2 Akor 4:16akhale munthu m’modzi watsopano...Aef 2:15kuti munthu wa Mulungu akhale...2 Tim 3:17chiwerengero chake ndi cha munthu...Chiv 13:18[onaninso: mwamuna]

MUNTHU (person)munthu woonongeka...Mas 15:4munthu waulesi adzavutika...Miy 19:15ndipo simuopa munthu...Mat 22:16koma kukhale munthu wobisika...1 Pet 3:4

MUVI (arrow)ndiwo muvi wakukupulumutsani...2 Maf 13:17muvi suthawitsa...Yob 41:28

apiringiza muvi wawo...Mas 11:2kapena muvi opita usana...Mas 91:5ndi muvi wakuthwa...Miy 25:18ndi muvi wakuphera...Yer 9:8polozetsa muvi...Malio 3:12

MUYAYA (eternal)Mulungu wa muyaya ndiye...Deut 33:27apita kwao kwa muyaya...Mlal 12:5ndiponso wa muyaya...2 Akor 4:17zosaoneka ndiye zamuyaya...2 Akor 4:18anthu, ndipo ndi yamuyaya...2 Akor 5:1[onaninso: wosatha]

MUYAYA (forever)kukhala moyo mpaka muyaya...Gen 3:22adakonda Israeli mpaka muyaya...1 Maf 10:9anakhala kwa muyaya pa mpando...Mas 29:10Mulungu, ndi wamuyaya...Mas 45:6ndiwe wansembe mpaka muyaya...Mas 110:4chikondi chake nchamuyaya...Mas 136:1nthawi zonse mpaka muyaya...Mas 145:1mfumu mpaka muyaya...Mas 146:10chuma sichikhala mpaka muyaya...Miy 27:24mukhulupirire Chauta mpaka muyaya...Yes 26:4adzakhalapo mpaka muyaya...Yes 40:8chidzakhala mpaka muyaya...Yes 51:6atumiki ao mpaka muyaya...Mali 3:31litamandike mpaka muyaya...Dan 2:20ngati nyenyezi mpaka muyaya...Dan 12:3Mulungu wathu mpaka muyaya...Mika 4:5ndi zanu kwa muyaya...Mat 6:13adzakhala ndi moyo mpaka muyaya...Yoh 12:34kwa Mulungu mpaka muyaya...Agal 1:5yonse mpaka muyaya...Aef 3:21alemekezedwa mpaka muyaya...Afil 4:20udzakhala mpaka muyaya...Aheb 1:8wakhala wangwiro kwa muyaya...Aheb 7:28wandiweyani mpaka muyaya...Yuda 13tsopano ndi mpaka muyaya...Yuda 25olamulira mpaka muyaya...Chiv 22:5

MIYESO (measures)m’nyumba yanu miyeso...Deu 25:14miyeso yosiyana ndi...Miy 20:10ndikuchenjerera nayo miyeso yonyenga...Amo 8:5

MIYESO (weight)miyeso ikhale miyeso...Deut 25:15[onaninso: cholemetsa, kulemera, muyeso]

MIZU (root)chitsiru chitamera mizu...Yob 5:3ngakhale mizu yake ikalambe...Yob 14:8zazimitsa mizu pansi...Yes 37:31zinali zosazika mizu...Mat 13:6[onaninso: muzu]

MIZU (roots)mizu yake inkazama...Ezek 31:7adzazika mizu ngati mtengo...Hos 14:5waumiratu wonse ndi mizu...Marko 11:20yofafa kawiri yozuka mizu...Yuda 12

MUYESO (line)muyeso wao wapitirira...Mas 19:4[onaninso: chingwe, mzere]

MUYESO (measure)mwala wa muyeso...Deut 25:15nayesa madzi miyeso...Yob 28:25muyeso wochepa umene.Mik 6:10

Page 108: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mzimu ndi muyeso...Yoh 3:34munthu aliyense muyeso...Aro 12:3muyese Kachisi wa...Chiv 11:1

MUYESO (weight)muyeso wonyenga umanyansa...Miy 11:1[onaninso: cholemetsa, kulemera, miyeso]

MUZU (root)kungofanafana ndi muzu...Deut 29:18kuti muzu wa Jese umene uima...Yes 11:10ngati muzu wa mtengo...Aro 11:16pakuti muzu wa zoipa zonse...1 Tim 6:10asakhale ngati muzu wowawa...Aheb 12:15Ine ndine muzu ndi mbadwa ya Davide...Chiv 22:16[onaninso: mizu]

MVERA (listen)mverani ine mosamalitsa...Yes 55:2Ambuye, mverani nimuchite...Dan 9:19akuopa Mulungu mverani...Mac 13:16[onaninso: kumva]

MVERA (obey)kuti ine nkumvera zimenezo...Eks 5:2wanu ndipo mudzamvera...Deut 4:30mukamvera malamulo a...Deut 11:27tidzamvera malamulo...Yos 24:24kapena kumvera mau...1 Sam 15:22ine adayamba kundimvera...Mas 18:44zidzachitika ngati mumveradi...Zek 6:15tiyenera kumvera Mulungu...Mac 5:29koma amvera chosalungama...Aro 2:8a munthu nkumamumvera...Aro 6:16muzimvera anakubala anu...Akol 3:20muziwamvera pazonse...Akol 3:22amene sadamvere uthenga...2 Ates 1:8muzimvera atsogoleri anu...Aheb13:17muzimvera amuna anu...1 Pet 3:1

MVERA (obeyed)mukamvera ndi mtima onse...Aro 6:17koma sanamvera Uthenga Wabwino...Aro 10:16Abrahamu adamvera...Aheb 11:8Sara yemwe ankamvera...1 Pet 3:6

MVERA (understand)kuti wina asamvere chinenedwe cha....Gen 11:7[onaninso: dziwa, dziwitsa, mvetsetsa, nzeru, zindikira]

MVETSA CHISONI (grieved)Yehova amamva chisoni...Gen 6:6mbadwo uwu unandimvetsa chisoni...Mas 95:10kumvetsa chisoni Mzimu wake Woyera...Yes 63:10ndi mkwiyo ndi kumva chisoni...Marko 3:5Petro anamva chisoni...Yoh 21:17[onaninso: lira misonzi, sauka mumzimu]

MVETSA CHISONI (grieve)kumvetsa ana a anthu chisoni...Mali 3:33musamvetse chisoni Mzimu Woyera...Aef 4:30

MVETSA (attention)mwana wanga, mvetsetsa...Miy 4:20[onaninso: penyerera, samalira]

MVETSA (understanding)ngakhale inunso simumvetsa...Mat 15:16kuti amvetse bwino...Luk 24:45adzakuthandiza kumvetsa...2 Tim 2:7ndi womvetsa zinthu...Yak 3:13[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kumvera, kuzindikira,

luntha, luso, nzeru]

MVETSA (understands)kwa munthu womvetsa...Miy 8:9koma munthu womvetsa...Miy 14:6palibe munthu womvetsa...Aro 3:11

MVETSA (understood)kodi simudamvetse...Yes 40:21mwazimvetsa zonsezi...Mat 13:51[onaninso: lingalira, phunzira, zindikirika]

MVETSETSA (understand)oipa samvetsetsa chiweruzo...Miy 28:5[onaninso: dziwa, dziwitsa, mvera, nzeru, zindikira]

MVULA (rain)anali asanagwetse mvula...Gen 2:5mvula inagwa pa dziko lapansi...Gen 7:12amagwetsa mvula pa dziko...Yob 5:10amalamulanso mvula kuti igwe...Yob 37:6Mulungu mudagwetsa mvula...Mas 68:9amapatsa nthaka mvula...Mas 147:8kapena mvula yimagwa...Miy 26:1ali ngati mvula yamkuntho...Miy 28:3mitambo idzabweranso mvula...Mlal 12:2mvula yatha ndipo yapitiriratu...Nyi 2:11amene amatipatsa mvula...Yer 5:24ndidzagwetsa mvula yoopsa...Ezek 38:22wakupatsani mvula yochuluka...Yow 2:23Mulungu wathu wopatsa mvula...Yer 5:24kukupatsani mvula yamyundo...Yow 2:23mvula sidzawagwera...Zek 14:17amagwetsera mvula anthu...Mat 5:45kudagwa mvula, mitsinje...Mat 7:25kumwamba amakupatsani mvula...Mac 14:17nthaka yolandira mvula kawirikawiri...Aheb 6:7kolimba kuti mvula isagwe...Yak 5:17atapempheranso, mvula idagwa...Yak 5:18[onaninso: vumbitsa]

MWALA WAPANGONDYA (cornerstone)anaika ndani mwala wake wapangondya...Yob 38:6wakhala mutu wapangondya...Mas 118:22woyesedwa mwala wapangondya...Yes 28:16unakhala mutu wa pangondya...Mat 21:42mwala wotsiriza wa pangondya...1 Pet 2:6

MWALA WAMPHERO (millstone)am’mangirire chimwala cha mphero...Mat 18:6kukula kwake ngati wamphero...Chiv 18:21

MWALA (capstone)mwala wotsiriza...Zek 4:7

MWALIRA (die)nthawi yobadwa ndi nthawi yomwalira...Mlal 3:2monga anthu onse amamwalira...1 Akor 15:22odala akufa akumwalira...Chiv 14:13[onaninso: ifa]

MWALIRA (died)munthu osauka uja anamwalira...Luk 16:22[onaninso: ifa)

MWAMBA (high)Yehova wamwambamwamba...Mas 47:2inu, Yehova muli m’mwamba...Mas 92:8wa m’mwambamwamba alamulira...Dan 4:17pokhala pako pamwamba...Obad 3[onaninso: kulu]

MWAMBO WOPEPESERA MACHIMO (atonement)

Page 109: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

adzachita mwambo wopepesera machimo...Eks 30:10tsiku limeneli padzakhala mwambo wopepesera machimo...Lev16:30kuti mudzichitira mwambo wopepesera machimo...Lev 17:11ndi tsiku lochita mwambo wopepesera machimo...Lev 23:28ndiponso nsembe zopepesera machimo...Neh 10:33[onaninso: kuchotsedwa, kufafaniza, kuyanjanitsa, ombola]

MWAMBO (custom)monga mwa mwambo...Mac 15:1[onaninso: makhalidwe]

MWAMBO (instruction)anyoza nzeru ndi mwambo...Miy 1:7gwira mwambo, osauleka...Miy 4:13imvani mwambo, mukhale...Miy 8:33wokonda mwambo akonda...Miy 12:1leka kumva mwambo...Miy 19:27lozetsa mtima wako ku mwambo...Miy 23:12[onaninso: chilangizo, langiza, malangizo]

MWAMUNA (husband)adapatsako mwamuna wake...Gen 3:6wa mwamuna wake...Miy 31:11ali ngati mwamuna wake...Yes 54:5mwamuna amene muli...Yoh 4:18mwamuna aliyense akhale...1 Akor 7:2mwamuna wachikunja...1 Akor 7:14udzampulumutsa mwamuna...1 Akor 7:16ndi mwamuna m’modzi yekha...2 Akor 11:2mwamuna ndi mutu wa mkazi...Aef 5:23mwamuna wa mkazi m’modzi...1 Tim 3:2[onaninso: mkwati]

MWAMUNA (man)pakuti mwamuna sakhala wa kwa mkazi...1 Akor 11:8[onaninso: munthu]

MWANA WAMKAZI (daughter)mwana mamwamuna kapena wamkazi...Owe 11:34kondwera kwambiri mwana wamkazi...Zek 9:9usaope mwana wamkazi wa Zioni...Yoh 12:15mwana wake wa mwana wamkazi wa Farao...Aheb 11:24

MWANA WANG’OMBE (calf)anachiyenga mwana wang’ombe...Eks 32:4anapanga mwana wang’ombe...Mas 106:19kuposa ng’ombe yonenepa pali udani...Miy 15:17ngati ng’ombe yaikazi yaing’ono...Hos 4:16mwana wang’ombe wako...Hos 8:5idzani naye mwana wang’ombe...Luk 15:23chinafanana ndi mwana wang’ombe...Chiv 4:7

MWANA WACHISAMBA (first born)mwana wanga wachisamba...Mas 89:27ndidzapereka mwana wanga wachisamba...Mika 6:7[onaninso: ana achisamba, wobadwa woyamba]

MWANA WAMDISO (apple)ngati kamwana ka m’diso...Deut 32:10Malamulo anga ngati mwana wa diso lako...Miy 7:2akhudza mwana wa m’diso lake...Zek 2:8

MWANA WA BURU (colt)ndi mwana wa buru wake...Gen 49:11ndi mwana wamphongo wa buru...Zek 9:9ndi pa kaburu...Mat 21:5zovala zao pamwamba pa mwana wa buruyo...Luk 19:35

MWANA (baby)mwana anayamba kutakataka...Luk 1:44mudzapeza mwana wakhanda wokutidwa...Luk 2:12

[onaninso: khanda]

MWANA (child)monga mwana amene amai ake...Mas 131:2ngakhale mwana amene amadziwika...Miy 20:11mwana muzimuphunzitsa njira yoti...Miy 22:6chifukwa mwana watibadwira...Yes 9:6mwana wamng’ono nkumaziweta...Yes 11:6pamene Israeli anali mwana...Hos 11:1nkubala mwana wamwamuna...Mat 1:23atatero adatenga mwana...Marko 9:36ufumu wa Mulungu ngati mwana...Marko 10:15kodi mwana ameneyu adzakhala munthu...Luk 1:66mwana uja Yohane ankakula...Luk 1:80pamene ine ndinali mwana...1 Akor 13:11maiyo adabala mwana...Chiv 12:5

MWANA (son)ndiwe mwana wanga...Mas 2:7pamene ndinali mwana...Miy 4:3mwana wanzeru amakondweretsa...Miy 10:1mwana wopusa amamvetsa...Miy 17:25nchiyani mwana wanga...Miy 31:2mwana watibadwira...Yes 9:6mwana wa mbandakucha...Yes 14:12ngati mwana wa Mulungu...Dan 3:25ali ngati mwana wopanda nzeru..Hos 13:13kapena mwana wa mneneri...Amo 7:14mwana amapatsa ulemu...Mal 1:6adzabala mwana wamwamuna...Mat 1:21uyu ndiye mwana wanga...Mat 3:17inu mwana wa Mulungu...Mat 8:29si mwana wa mmisiri...Mat 13:55ndithudi ndinu mwana wa...Mat 14:33mwana wa Mulungu wamoyo...Mat 16:16adawatumira mwana wake...Mat 21:37ndi mwana wa Davide...Mat 22:42angakhale mwana wakenso...Mat 22:45mumsandutsa mwana wa gehena...Mat 23:15kwa mwana wa munthu...Mat 24:37ankati, ndine mwana wa...Mat 27:43munthuyu adalidi mwana wa...Mat 27:54Yesu Khristu, mwana wa...Marko 1:1adzatchedwa mwana wa Mulungu...Luk 1:32anali mwana wamwamuna...Luk 7:12mukakhala mwana wa mtendere...Luk 10:6kutchedwanso mwana wanu...Luk 15:19ndi mwana wa Abrahamu...Luk 19:9mwana mmodzi yekha...Yoh 1:18kuti Mwana wa Mulungu ndi Yemweyu...Yoh 1:34wokhulupirira mwanayo...Yoh 3:18mwanane sindingathe kuchita...Yoh 5:19nthawi zonse, koma mwana...Yoh 8:35nkukhulupirira mwana wa...Yoh 9:35ndati ndine mwana wa...Yoh 10:36mai, nayu mwana wanu...Yoh 19:26Yesu Khristu ndi mwana...Mac 8:37Yesuyo ndi mwana...Aro 1:4wonena za mwana wake...Aro 1:9Mulungu anatumiza Mwana wake...Aro 8:3potuma mwana wakewake...Aro 8:32mwana wa Mulungu...1 Akor 15:28kukhulupirira mwana wa...Agal 2:20adatuma mwana wake...Agal 4:4kapolo ai, koma mwana...Agal 4:7pakudziwa mwana wa...Aef 4:13mwana wanga mwa...Fil 10Iwe ndiwe mwana wanga...Aheb 1:5ngati mwana wolamulira...Aheb 3:6ngakhale anali mwana...Aheb 5:8ali ngati mwana wa...Aheb 7:3anakana kutchedwa mwana wake...Aheb 11:24

Page 110: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

uyu ndi mwana wanga...2 Pet 1:17aliyense wokana mwana...1 Yoh 2:23amene amakhulupirira mwana ...1 Yoh 5:10ngati mwana wa munthu...Chiv 1:13

MWANO (blaspheme)ndi kuwakakamiza anene za mwano...Mac 26:11aphunzire kusalankhula za mwano...1 Tim 1:20sachitira mwano iwowa...Yak 2:7kuchitira mwano dzina lake...Chiv 13:6[onaninso: nyoza]

MWANO (blasphemed)dzina langa lichitidwa mwano...Yes 52:5anamchitira mwano iye...Mat 27:39anamchitira iye mwano...Luk 23:39dzina la Mulungu lichitidwa mwano...Aro 2:24zisachitidwe mwano...1 Tim 6:1anachitira mwano dzina la Mulungu...Chiv 16:9[onaninso: nyoza, tonzedwa]

MWANO (blasphemes)wakulichitira mwano dzina la Yehova...Lev 24:16uyu achitira Mulungu mwano...Mat 9:3

MWANO (blasphemies)za umboni wonama, zamwano...Mat 15:19zomchitira Mulungu mwano...Luk 5:21zazikuru ndi zamwano...Chiv 13:5

MWANO (blasphemy)koma chamwano cha pa...Mat 12:31achitira Mulungu mwano...Mat 26:65chodzala ndi maina a mwano...Chiv 17:3

MWAZA (disperse)ndi kuwamwaza m’maiko...Ezek 20:23

MWAZA (scatter)amaononga ndi kumwaza...Yer 23:1ochita zoipa adzamwazikana...Mas 92:9ngati nkhosa zomwazikana...Yer 50:17amamwaza chipale...Mas 147:16ameneyo ndi womwaza...Mat 12:30[onaninso: balalitsa]

MWAZI (blood)mau a mwazi wa mphwako...Gen 4:10amene akhetsa mwazi...Gen 9:6mkwati wanga wa mwazi...Eks 4:25wanyama ukhala m’mwazi...Lev 17:11mwazi wake ndiwo moyo...Lev 17:14usakwirire mwazi wanga...Yob 16:18m’mwazi mwanga muli...Mas 30:9namtsutsa wa mwazi...Mas 94:21manja anu adzala mwazi...Yes 1:15lidzavumbulutsa mwazi wake...Yes 26:21mwezi udzasanduka mwazi...Yow 2:31mwazi wanga wa pangano...Mat 26:28munda wa mwazi...Mat 27:8mwazi wake uli pa ife...Mat 27:25pangano latsopano m’mwazi...Luk 20:28sanabadwa ndi mwazi...Yoh 1:13ndi kumwa mwazi wanga...Yoh 6:54anaugula ndi mwazi...Mac 20:28chikhulupiriro cha m’mwazi...Aro 3:25olungama ndi mwazi wake...Aro 5:9maomboledwe mwa mwazi...Aef 1:7mukhale pafupi m’mwazi...Aef 2:13sitilimbana nawo mwazi...Aef 6:12mtendere mwa mwazi...Akol 1:20uwu ndi mwazi wa...Aheb 9:20wopanda kukhetsa mwazi...Aheb 9:22

zosayeretsedwa ndi mwazi...Aheb 9:22ndi mwazi wa Yesu...Aheb 10:19kuwaza kwa mwazi wa Yesu...1 Pet 1:2koma ndi mwazi wamtengo...1 Pet 1:19ndipo mwazi wa Yesu...1 Yoh 1:7kumachimo athu ndi mwazi...Chiv 1:5ndi mwazi wanu anthu...Chiv 5:9naziyeretsa m’mwazi wa...Chiv 7:14iye chifukwa cha mwazi...Chiv 12:11chowazidwa mwazi...Chiv 19:13

MWAZI (bloodshed)kumlandu wa mwazi...Mas 51:14dziko ladzala ndi mwazi...Ezek 9:9amanga Ziyoni ndi mwazi...Mik 3:10

MWEZI (moon)sipadzakhala mwezi...Mas 72:7dzuwa ndi mwezi zada...Nyi 6:10dzuwa ndi mwezi zada...Yow 2:10lidzadetsedwa ndi mwezi...Marko 13:24

MWINJIRO (cloak)umlole atengenso ndi mwinjiro wako...Mat 5:40mudzazipindapinda ngati mwinjiro...Aheb 1:12[onaninso: maraya]

MWINJIRO (robe)chiweruzo changa chinanga mwinjiro...Yob 29:14[onaninso: maraya, mkanjo]

MZERE (line)lemba mzere ndi mzere...Yes 28:10[onaninso: chingwe, muyeso]

MZINDA (city)tsono Kaini adamanga mzinda...Gen 4:17imasangalatsa anthu a mu mzinda...Mas 46:4osapeza njira yopita ku mzinda...Mas 107:4akapanda kulonda nawo mzinda...Mas 127:1kumaso kwa mzinda...Miy 8:3mzinda umene kale unali wokhulupirika...Yes 1:21mzika za mzinda wopatulika...Yes 48:2mzinda wa Yerusalemu...Mali 1:1kuumvera chisoni mzinda...Yon 4:11umenewo ndiwo mzinda...Zef 2:15Yerusalemu, mzinda wopanduka...Zef 3:1iye adawakonzera mzinda...Aheb 11:16ndiponso ku mzinda wa Mulungu...Aheb 12:22paja ife tilibe mzinda wokhazikika...Aheb 13:14adzaupondereza mzinda woyerawo...Chiv 11:2ndi mzinda umene Mulungu amaukonda...Chiv 20:9tsono ndinaona mzinda...Chiv 21:2linga la mzindawo linali..Chiv 21:18kapena mwezi ziziwala pa mzindapo...Chiv 21:23kulowa mumzinda kudzera...Chiv 22:14

M’MBUYO (back)Yordano anabwerera m’mbuyo...Mas 114:3ndi kunditaya pambuyo pako...Ezek 23:35nayang’ana za kumbuyo...Luk 9:62anabwerera m’mbuyo, nagwa...Yoh 18:6anagwa chambuyo...1 Sam 4:18mthunzi m’mbuyo...2 Maf 20:11[onaninso: msana]

M’MISIRI WA ZITSULO (blacksmith)m’misiri wa zitsulo amatenga chitsulo...Yes 44:12[onaninso: wachipala]

M’MISIRI (builder)

Page 111: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

monga m’misiri waluso...1 Akor 3:10m’misiri woganiziratu mamangidwe...Aheb 11:10

M’MISIRI (expert)wakuphunzitsa amisiri onse...Gen 4:22chotero m’misiri wa mitengo...Yes 41:7m’misiri wa mitengo atambalitsa...Yes 44:13[onaninso: katswiri, waluso]

M’MWAMBA (above)la za m’mwamba ndi za padziko...Afil 2:9[onaninso: kumwamba, pamwamba, posa]

N

NAAMANI (Naaman)wamkulu wa asirikali mu gulu lankhondo la Siriya...2 Maf5:1-11anachiritsidwa khate lake...2 Maf 5:14-17ananenedwa ngati chitsanzo ndi Khristu...Luk 4:27

NABALA (Nabal)anakana pempho la Davide...1 Sam 25:2-12anathawa mkwiyo wa Davide koma anafa ndi nthenda yofaziwalo...1 Sam 25:13-39

NABOTI (Naboth)anaphedwa chifukwa cha munda wamphesa wake...1 Maf21:1-16kuphedwa kwake kunabwezeredwa...1 Maf 21:17-25

NADABU (Nadab)mwana wamwamuna wamkulu pa ana anayi amuna aAroni...Eks 6:23anatenga gawo posindikiza chipangano...Eks 24:1,9-12anakhala wansembe...Eks 28:1anaonongedwa ndi moto...Lev 10:1-7— mfumu ya Israeli...1 Maf 14:20inaphedwa ndi Basa...1Maf 15:25-31

NADZICHEPETSA (humbled)nadzichepetsa kwambiri pamaso...2 Mbir 33:12anadzichepetsa yekha...Afil 2:8

NAFUTALI (Naphtali)mwana wa Yakobo kudzera mwa Biliha...Gen 30:1-8analandira madalitso a Yakobo...Gen 49:21,28fuko lake linawerengedwa...Num 1:42,43dera linapatsidwa kwa...Yos 19:32-39linalowa gulu lankhondo la Gideoni...Ower 7:23anathiridwa nkhondo ndi Beni-Hadadi ndi Tigilati Pileza...1Maf 15:20; 2 Maf 15:29uneneri wa kuwala kwakukulu mwa;unakwaniritsidwa mu utumiki wa Khristu...Yes 9:1-7; Mat4:12-16

NAHASI (Nahash)mfumu ya Aamoni; inapanga malamulo osatheka...1 Sam11:1-15

NAHORI (Nahor)agogo aamuna a Abrahamu...Gen 11:24-26— mwana wa Tera; mbale wake wa Abrahamu...Gen 11:17

NAHUMU (Nahum)mneneri wa Yuda onenera zokhudza Ninive...Nah 1:1

NAILO (Nile)ana a chiyuda anaponyedwamo...Eks 1:22Mose anabisidwamo...Eks 2:3-10madzi ake, anasanduka magazi...Eks 7:14-21ananenedwa m’mauneneri...Yes 19:5-8; 23:3; 27:12; Yer

46:7-9; Amosi 9:5

NAINI (Nain)mudzi wa kuzambwe kwa Nazareti;Yesu anaukitsa mwana wa mzimai wamasiye kumeneku...Luk7:11-17

NAMA (lie)sindiye munthu kuti aname...Num 23:19umene Mulungu wosanamayo...Tit 1:2ndipo musamanama potsutsana nacho...Yak 3:14mboni yonama...Miy 19:5[onaninso: bodza, namiza, namizira]

NAMA (lying)wolungama ada mau onama...Miy 13:5musamakhulupirire mau onama...Yer 7:4mwa ichi, mutataya zonama, lankhulani...Aef 4:25ndi zizindikiro ndi zozizwa zonama...2 Ates 2:9[onaninso: bodza, gona, khala]

NAMIZA (lie)musamanamizana wina ndi mnzake...Akol 3:9sudanamiza anthu koma...Mac 5:4[onaninso: bodza, nama, namizira]

NAMIZIRA (lie)sindidzanamizira Davide...Mas 89:35[onaninso: bodza, nama, namiza]

NAMZEZE (swallow)ndi namzeze alikuuluka...Miy 26:2ndinalankhula-lankhula ngati namzeze...Yes 38:14ndi namzeze ndi chingaru ziyang’anira...Yer 8:7[onaninso: meza]

NANGULA (anchor)chiyembekezo chimenechi tilinacho ngati nangula...Aheb 6:19

NAOMI (Naomi)mkazi wamasiye wa ku Elemeleki...Rut 1:1-3anabwerera ku Betelehemu ndi Rute...Rut 1:14-19anakonza za ukwati wa Rute ndi Bowazi...Rut 3,4

NATANAELE (Nathanael)m’modzi wa ophunzira ake a Yesu...Yoh 1:45-51

NATANI (Nathan)mwana wa Davide...2 Sam 5:14mneneri yemwe mndandanda wa banja la Marialinadzerera...Zek 12:12— mneneri nthawi ya Davide ndi Solomoni...1 Mbir 29:29anaonetsera chifuniro cha Mulungu kwa Davide...2 Sam 7:2-29anadzudzula tchimo la Davide...2 Sam 12:1-15anavumbulutsira chiwembu cha Adoniya...1 Maf 1:10-46

NAYOTI (Naioth)sukulu ya aneneri ku Rama...1 Sam 19:18,19,22,23

NAZARETI (Nazareth)mzinda wa makolo ake a Yesu...Mat 2:23kwao koyamba kwa Yesu...Luk 2:39-51Yesu anakanidwa nao...Luk 4:16-30Mzinda wa ku Galileya...Yoh 1:46

NDALAMA (coin)ali nazo ndalama zasiliva khumi...Luk 15:8[onaninso: kobiri]

NDALAMA (money)ndalama zake sakongoletsa...Mas 15:5moyo, ndipo ndalama zivomera...Mlal 10:19

Page 112: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mudzaomboledwa opanda ndalama...Yes 52:3ndi osowa ndalama idzani...Yes 55:1magome a osintha ndalama...Mat 21:12nakumba pansi, nabisa ndalama...Mat 25:18kuti adzampatsa ndalama...Marko 14:11musanyamule thumba la ndalama...Luk 10:4opanda thumba la ndalama...Luk 22:35ndi akusinthana ndalama...Yoh 2:14ndalama yako itayike nawe...Mac 8:20ndi wosakonda ndalama...1 Tim 3:3ndiwo chikondi cha pa ndalama...1 Tim 6:10wokonda kudya phindu la ndalama...Tit 1:7

NDEKHANDEKHA (desolate)pakuti ndiri ndekhandekha...Mas 25:16[onaninso: bwinja, wosiyidwa]

NDENDE (chains)ine m’ndende za Uthenga Wabwino...Fil 13anawaponya kundende...2 Pet 2:4[onaninso: maunyolo, nkhata, nsinga, zomangira]

NDENDE (prison)nakamtsekera mndende...Gen 39:20tulutseni mndende...Mas 142:7adzamasula akaidi mndende...Yes 42:7ndiponso kwa am’ndende...Yes 61:1udzimponya mndende...Yer 29:26Yohane Mbatizi anali mndende...Mat 11:2ndidaali mndende...Mat 25:36mizimu imene inali mndende...1 Pet 3:19nadzakuponyani mndende...Luk 21:12

NDEU (contentions)nyanga, madano, ndeu...Agal 5:20[onaninso: mikangano]

NDEVU (beard)m’mphepete mwa ndevu zanu...Lev 19:27Yoabu anagwira ndevu...2 Sam 20:9akutsikira ku ndevu...Mas 133:2[onaninso: chowa]

NDINE (am)Ndine yemwe ndili...Eks 3:14Ndine woyamba...Yes 44:6ndiri nawo...Mat 18:20chopatsa moyo ndine...Yoh 6:35ndine kuwala kounika...Yoh 8:12ndine wochokera Kumwamba...Yoh 8:23Ine ndilipo...Yoh 8:58khomo ndine...Yoh 10:9Ine ndine Mbusa Wabwino...Yoh 10:11wopatsa moyo ndine...Yoh 11:25ndine njira, choonadi...Yoh 14:6ndili ine amene ndili...1 Akor 15:10

NDODO YAUFUMU (scepter)ndodo yaufumu sidzachoka...Gen 49:10ndodo yaufumu idzadzuka...Num 24:17ndodo yachifumu ya ufumu...Mas 45:6ngati ndodo yachifumu...Aheb 1:8

NDUNA (princes)amange nduna zake iye...Mas 105:22nduna zomwe zinakhala zondineneza...Mas 119:23zinduna ndi oweruza onse...Mas 148:11[onaninso: akalonga, akuru]

NDUNGUNDUNGU (dregs)nadzagugudiza mpaka ndungundungu zake...Mas 75:8[onaninso: nsenga]

NDUWIRA ZACHIFUMU (crowns)ndi panyanga zache nduwira zachifumu khumi...Chiv

13:1ndi pamutu pache pali nduwira zachifumu zambiri...Chiv 19:12[onaninso: akorona]

NEBO (Nebo)mulungu wa Chibabiloni...Yes 46:1— pamwamba pa Pisiga, Mose anafera kumeneko...Deut 32:49;

34:1,5

NEBUKADINEZARA (Nebuchadnezzar)ulamuliro wa banja la chifumu wa ku Babiloni... (605-562BC);anatenga Ayuda ku ukapolo ku Babiloni...Dan 1:1-3anagonjetsa kuukira kwa Yehoyakini...2 Maf 24:10-17anaononga Yerusalemu; anagwira Zedekiya...Yer 39:5-8Uneneri wokhudza...Yes 14:4-27;Yer 21:7-10; 25:8,9; 27:4-11;32:28-36; 43:10-13;Ezek 26:7-12

NEBUZARADANI (Nebuzaradan)wamkulu wa nkhondo wa Nebukadinezara pa nthawi yoonongaYerusalemu...2 Maf. 25:8-20anamteteza Yeremiya...Yer 39:11-14

NEHEMIYA (Nehemiah)wopereka chikho kwa mfumu Atasesesi;anapempherera kubwezeretsedwanso kwa Yerusalemu...Neh1:4-11mfumu inamuloleza kumanga malinga/makoma...Neh 2:1-8anagonjetsa otsutsana naye nakwaniritsa kumanganso kwaYerusalemu...Neh 4-6anasankhidwa ubwanamkubwa...Neh 5:14anakhalira limodzi ndi Ezara mu kubwezeretsakupembedza...Neh 8-10analemba anthu, ansembe ndi alembi...Neh 11:1-12:26anapereka malinga...Neh 12:27-43anabwerera ku Yerusalemu ndi kukakhazikitsa zinthuzosinthidwa...Neh 13:4-31

NENEPA (fatted)ng’ombe ndi nyama zina zonenepa...Mat 22:4apha mwana wang’ombe wonenepa...Luk 15:27

NENERA (plead)iye amene amnenera mlandu...Ower 6:31mundinenere mlandu kwa anthu...Mas 43:1[onaninso: pempha, pemphero, tsutsana, weruza]

NENERA (prophesied)Mzimu pa iwowa ananenera...Num 11:25ndi iwo, koma ananenera...Yer 23:21Ambuye kodi sitinanenera mau m’dzina lanu...Mat 7:22sitinanenera mau m’dzina lanu...Mat 11:13anamwali amene ananenera...Mac 21:9wakunenera aposa wakulankhula malilime...1 Akor 14:5

NENEZA (accusation)analembera chowaneneza...Ezara 4:6kuti akapeze chomneneza...Luk 6:7usalandira chomnenera...1 Tim 5:19sawaneneza kwa...2 Petr 2:11

NENEZA (accuse)ndipo anayamba kumnenera...Luk 23:2Ine ndidzakunenezani...Yoh 5:45

NENEZA (accused)naneneza Ayuda...Dan 3:8ndipo pakumneneza...Mat 27:12wonenera wa abale...Chiv 12:10

Page 113: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

NENEZA (accusing)ndi mnzake anenezana...Aro 2:15

NENEZA (testify)ndipo machimo athu otineneza ife...Yes 59:12[onaninso: chitira umboni]

NETINIMU (Nethinim)atumiki a Alevi...Ezara 8:20kochokera kwa:Agibione...Yos 9:23-27antchito okakamizidwa a Solomoni...1 Maf 9:20,21ananenedwa ku...1 Mbir 9:2; Ezara 2:43-54; 7:24; 8:17;Neh 3:31; 7:46-60,73; 10:28,29; 11:21

NGAKHALE (even)ngakhale poseka mtima...Miy 14:13ngakhale mwana yemwe...Miy 20:11onama ngakhale pakati pa Aisraele...2 Pet 2:1

NGAMILA (camel)nkwapafupi kuti ngamila...Mat 19:24koma ngamila mum’meza...Mat 23:24

NGONGOLE (owe)musakhale ndi ngongole ina iriyonse...Aro 13:8paja iweyo ngongole yako...Fil 19[onaninso: kongola]

NGULI (cymbal)kapena nguli yolira...1 Akor 13:1

NGWIRO (blameless)mukhale angwiro ndi Yehova...Deut 18:13ndipo munthuyu anali wangwiro...Yob 1:1mtima wanga ukhale wangwiro...Mas 119:80[onaninso: khala wosalakwa, opanda chilema, panda chilema]

NGWIRO (perfect)munthu wolungama ndi wangwiro...Gen 6:9wadziwitsa mwangwiro ali...Yob 36:4Mulungu ndiye wangwiro mnjira...Mas 18:30unali wangwiro mnjira zako...Ezek 28:15inu mukhale angwiro...Mat 5:48ngati ufuna kukhala wangwiro...Mat 19:21kuti akhale angwiro mwa mmodzi...Yoh 17:23chokondweretsa ndi changwiro...Aro 12:2pamene changwiro chafika...1 Akor 13:10kuti akhale wangwiro mwa Khristu...Akol 1:28olungama oyesedwa angwiro...Aheb 12:23chiri chonse changwiro zichokera...Yak 1:17iye ndiye munthu wangwiro...Yak 3:2wamanthayo sakhala wangwiro...1 Yoh 4:18

NGWIRO (well)ana akazi ambiri anachita mwangwiro...Miy 31:29[onaninso: bwino,chitsime, komera, limba, pulumutsa]

NG’ANJO YA MOTO (furnace)nakutulutsani m’ng’anjo ya moto...Deut 4:20ndakuyesa iwe m’ng’anjo ya masautso...Yes 48:10m’kati mwa ng’anjo yotentha ya moto...Dan 3:6adzawataya iwo mng’anjo ya moto...Mat 13:42ngati utsi wa ng’anjo yayikulu...Chiv 9:2

NG’ANJO (oven)monga m’mene ng’anjo yamoto...Mas 21:9ngati chiputu mng’anjo...Malak 4:1[onaninso: moto]

NG’OMBE (bull)sindidzatenga ng’ombe...Mas 50:9monga mwana wa ng’ombe...Yer 31:18mwazi wa ng’ombe za mphongo...Yes 1:11ndi ng’ombe za mphongo...Aheb 9:13

NG’OMBE (cattle)zofunkha zake ndi ng’ombe...Yos 8:2[onaninso: zoweta]

NG’OMBE (ox)musamapunamiza ng’ombe popuntha...Deut 25:4ng’ombe idziwa mwini wake...Yes 1:3zinali nayo nkhope ya ng’ombe...Ezek 1:10samaimasula ng’ombe yake kapena...Luk 13:15usapunamitsa ng’ombe...1 Akor 9:9[onaninso: njati]

NG’ONA (monster)wandimeza ngati ng’ona...Yer 51:34ng’ona yaikulu yakugona...Ezek 29:3

NG’ONO (little)ankhandwe, ngakhale ang’ono...Nyi 2:15tiri ndi mlongo wathu wamng’ono...Nyi 8:8kuno pang’ono pano...Yes 28:10Betelehemu Efrata, ndi wamng’ono...Mika 5:2koma taonani pang’ono...Hag 1:9pakuti ndinakwiya pang’ono...Zek 1:15adzamwetsa m’modzi wa ang’ono...Mat 10:42iwe wokhulupirira pang’ono...Mat 14:31anamkhululukira pang’ono...Luk 7:47khulupirika pa zazing’ono...Luk 19:17chizolowezi chathu chipindula pang’ono...1 Tim 4:8

NIKANORE (Nicanor)m’modzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:1-5

NIKODEMO (Nicodemus)mfarisi, anakambirana ndi Yesu...Yoh 3:1-12anatsutsa kusowa chilungamo mu mlandu wa Yesu...Yoh7:50-52anabweretsa mphatso kudzodza thupi la Yesu...Yoh 19:39,40

NIKOLASI (Nicolas)m’modzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:5

NIMIRODI (Nimrod)chidzukulu cha Hamu...Gen 10:6-12

NINIVE (Niniveh)mzinda waukulu wa Asiriya...2 Maf 19:36Yona analalikirako; anthu ake analapa...Yon 3:1-10; Mat 12:41uneneri woukhudza...Nah 2:13-3:19; Zef 2:13-15

NJATI (ox)njati idzavomera kukutumikira...Yob 39:9ukhoza kumanga njati...Yob 39:10monga nsona wa njati...Mas 29:6nyanga yanga ngati ya njati...Mas 92:10[onaninso: ng’ombe]

NJENJETE (moth)chovala, njenjete zidzawadya...Yes 50:9pamene njenjete ndi zimbiri...Mat 6:19

NJERWA (bricks)udzu wa njerwa...Eks 5:7pa maguwa a njerwa...Yes 65:3ndipo muumbe njerwa...Nah 3:14tiyeni tiumbe njerwa...Gen 11:3chiwerengero cha njerwa...Eks 5:8

Page 114: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

koma chiwerengero cha njerwa...Eks 5:18ngakhale njerwa zagumuka...Yes 9:10

NJINGA (wheels)kuyenda kwa njinga za magareta...Nah 3:2[onaninso: mikombero]

NJIRA (highway)koma njira ya oongoka mtima...Miy 15:19konzani njira ya Yehova...Yes 40:3konzani njira ya anthu...Yes 62:10

NJIRA (path)njira ya mgodi imeneyi...Yob 28:7njira ya kumoyo...Mas 16:11munditsogolere mnjira yosalala...Mas 27:11njira ya anthu okondweretsa...Miy 4:18njira pakati pa madzi...Yes 43:16

NJIRA (paths)amanditsogolera mnjira za...Mas 23:3mundidziwitse njira zanu...Mas 25:4imakudzeretsa mnjira za chilungamo...Miy 3:17ndidzawaperekeza panjira...Yes 42:16anayenda mnjira zokhotakhota...Yes 59:8ongolani njira yoti...Mat 3:3muziyenda mnjira zoongoka...Aheb 12:13

NJIRA (road)zikhale njira zakupitamo...Yes 51:10umo adaonekera Ambuye m’njira...Mac 9:27[onaninso: mseu]

NJIRA (way)kuwadziwitsa njira imene ayenera...Eks 18:20ndirikumuka njira ya dziko lonse...Yos 23:14ndidzakulangizani njira yabwino...1 Sam 12:23njira yake iri yabwino...2 Sam 22:31munthu wa njira yobisika...Yob 3:23adziwa njira ndilowayi...Yob 23:10iri kuti njira yomukira...Yob 38:19ndipo mungatayike m’njira...Mas 2:12mundiphunzitse njira yanu...Mas 27:11njira yao yino ndiyo kupusa...Mas 49:13njira yanu idziwike padziko lapansi...Mas 67:2njira yanu inali m’nyanja...Mas 77:19mchipululu mopanda njira...Mas 107:40ndinasankha njira yokhulupirika...Mas 119:30ndimatsata njira yoipa...Mas 139:24mlonda wa njira zolungama...Miy 2:8njira ya anthu oipa...Miy 4:19zidzudzulo za mwambo ndizo njira...Miy 6:23pali njira ina yooneka...Miy 14:12monga sudziwa njira ya mphepo...Mlal 11:5panjira padzakhala zoopsa...Mlal 12:5mumasalaza njira ya munthu...Yes 26:7mau akukulozerani njira...Yes 30:21adapanga njira panyanja...Yes 43:16woipa asiye njira yake...Yes 55:7ndidziwa kuti njira ya munthu...Yer 10:23mtima umodzi ndi njira imodzi...Yer 32:39mukuti Njira ya Ambuye njosayenera...Ezek 18:25akuti Njira ya Ambuye siiyenera...Ezek 33:17napotoza njira ya ofatsa...Amo 2:7njira ya Yehova iri m’kamvumvulu...Nah 1:3akandikonzere njira...Mal 3:1njira yake ndi yofumbula...Mat 7:13njira yake ndiyosautsa...Mat 7:14ikakonzeretu njira...Mat 11:10ndipo muphunzitsa njira ya Mulungu...Mat 22:16njira yake mukuidziwa...Yoh 14:4ineyo ndine njira...Yoh 14:6

akukulalikirani njira ...Mac 16:17njira ya Mulungu...Mac 18:26ndikuwonetseni njira yopambana...1 Akor 12:31adatitsekulira njira...Aheb 10:20adasiya njira yolungama...2 Pet 2:15akadakhala osadziwa njira...2 Pet 2:21adatsata njira ya Kaini...Yuda 11[onaninso: mayendedwe]

NJIRA (ways)njira zake zonse...Deut 32:4ndipo sadziwa njira zake...Yob 24:13mundidziwitse njira zanu...Mas 25:4mundidziwitse njira zanu...Mas 51:13Aisraeli akadayenda mnjira...Mas 81:13ndikadakonda kuti njira...Mas 119:5ndikamalingalira njira zanga...Mas 119:59ali wolungama m’njira zake...Mas 145:17njira zake zonse...Miy 5:21njira za munthu zikakonda Yehova...Miy 16:7adzatiphunzitsa za njira zake...Yes 2:3njira zanu sizili njira zanga...Yes 55:8kumene kuli njira zakale...Yer 6:16konzani njira zanu...Yer 7:3tisanthule ntiyese njira zathu...Mali 3:40ndi njira zanu zonse...Dan 5:23njira zake nzachikhalire...Hab 3:6njira zake ndani...Aro 11:33wosinkhasinkha pa njira zake zonse...Yak 1:8adanyoza njira za choona...2 Pet 2:2njira zanu nzolungama...Chiv 15:3[onaninso: machitidwe]

NJIRU (envy)za kunyenga ndi za njiru...Aro 1:29okhala mdumbo ndi njiru...Tit 3:3[onaninso: kaduka, nsanje]

NJIWA (dove)akadandipatsa mapiko onga a njiwa...Mas 55:6[onaninso: nkhunda]

NJOKA (serpent)njoka inali yochenjera...Gen 3:1njoka ndiyo idandinyenga...Gen 3:13upange njoka ya mkuwa...Num 21:8ululu wonga wa njoka...Mas 58:4mkango ndi njoka...Mas 91:13likhale ngati la njoka...Mas 140:3imayendera njoka...Miy 30:19kuseweretsa njoka...Mlal 10:11mtundu wa njoka...Yes 14:29ndi kubaya chinjoka...Yes 51:9iye nkumpatsa njoka...Mat 7:10njoka pamtengo...Yoh 3:14chinjoka chachikulu...Chiv 12:9ululu wa njoka...Deut 32:33ochenjera ngati njoka...Mat 10:16kuti muziponda njoka...Luk 10:19

NJUCHI (bee)adzabwera ambiri ngati njuchi...Yes 7:18

NKHAKA (cucumbers)mnkhaka ndi mavwendi...Num 11:5m’munda wa mnkhaka...Yes 1:8

NKHALAMBA (elder)nkhalamba ndi wolemekezeka...Yes 9:15[onaninso: mkulu]

NKHALANGO (forest)

Page 115: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

nyama iliyonse ya m’nkhalango...Mas 50:10kukula kwake kwa nkhalango...Yak 3:5

NKHALI (pot)ngati wa mnkhali...Yob 41:20[onaninso: mbiya, mtsuko]

NKHANDWE (fox)a chimanga, ikakwerako nkhandwe...Neh 4:3pitani kauzeni nkhandweyo...Luk 13:32Samisoni adakagwira nkhandwe...Ower 15:4nkhandwe zing’ono zing’ono zimene...Nyi 2:15nkhandwe zili ndi michembo yake...Luk 9:58

NKHANZA (cruel)chifundo cha oipa ndi nkhanza...Miy 12:10[onaninso: nkharwe, wolemera]

NKHARWE (cruel)chifukwa kunali kwankharwe...Gen 49:7[onaninso: nkhanza, wolemera]

NKHATA (chains)akongola ndi nkhata ya tsitsi...Nyi 1:10[onaninso: maunyolo, ndende, nsinga, zomangira]

NKHAWA (anguish)nditenga nkhawa chifukwa cha...Mas 38:18[onaninso: chipsinjo, kusauka, kusautsika, kuwawa mtima]

NKHAWA (anxieties)pamene nkhawa zikundichulukira...Mas 94:19nkhawa iweramitsa mtima...Miy 12:25adzadya mkate wawo ndi nkhawa...Ezek 12:19ndi kuda nkhawa angathe...Luk 12:29musadere nkhawa konse...Afil 4:6

NKHAWA (anxiety)nkhawa iweramitsa mtima wa munthu...Miy 12:25adzadya mkate wao ndi nkhawa...Ezek 12:19

NKHAWA (burden)umsenze Yehova nkhawa zako...Mas 55:22[onaninso: chinthenda, katundu, kukoka, lemetsa]

NKHAWA (care)pasakhale zokudetsani nkhawa...1 Akor 7:32[onaninso: samala]

NKHAWA (cares)kutaya pa iye nkhawa...1 Pet 5:7atsamwitsidwa ndi nkhawa...Luk 8:14[onaninso: samala]

NKHAWA (conflict)mudziwe nkhawa imene ndili nayo...Akol 2:1[onaninso: chilimbano]

NKHOKWE (barns)motere nkhokwe zako...Miy 3:10nkhokwe zapasuka...Yow 1:17ndidzapasula nkhokwe zanga...Luk 12:18kodi mbeu ikali mnkhokwe...Hag 2:19musonkhanitse tirigu mu nkhokwe yanga...Mat 13:30kapena nkhokwe...Luk 12:24sizimatutira m’nkhokwe...Luk 12:24

NKHONDO (battle)pakuti Yehova ndiye mwini nkhondo...1 Sam 17:47mchuno kunkhondoyo...Mas 18:39chifukwa cha tsiku la nkhondo...Miy 21:31olimba sapambana m’nkhondo...Mlal 9:11

amene abweza nkhondo pachipata...Yes 28:6phokoso la nkhondo lili m’dziko muno...Yer 50:22adzadzikonzera ndani ku nkhondo?...1 Akor 14:8anakula mphamvu ku nkhondo..Aheb 11:34ku nkhondo ya tsiku lalikulu...Chiv 16:14

NKHONDO (fight)kodi udzapita nane kunkhondo...1 Maf 22:4uzimenya nkhondo yabwino...1 Tim 6:12ndamenya nkhondo yabwino...2 Tim 4:7kodi nkhondo zimachokera...Yak 4:2[onaninso: menya]

NKHONDO (fights)zichokera kuti nkhondo...Yak 4:1[onaninso: menya]

NKHONDO (war)kuli phokoso la nkhondo...Eks 32:17ndi kudzikonza kunkhondo...Num 32:20aphunzitsa manja anga nkhondo...2 Sam 22:35nthawi yomenyana nkhondo...Yob 38:23ngakhale gulu la nkhondo...Mas 27:3iwo amafuna nkhondo...Mas 120:7usamenye nkhondo...Miy 20:18kuti ukamenye nkhondo...Miy 24:6sidzaphunziranso kumenya nkhondo...Yes 2:4ndiponso nkhondo yoopsa...Yes 21:15kopanda nkhondo...Yer 42:14imeneyo idachita nkhondo...Dan 7:21osaganizako za nkhondo...Mika 2:8popita kunkhondo kukakumana...Luk 14:31msirikali ndani achita nkhondo...1 Akor 9:7nkhondo zimachokera kuti...Yak 4:1nkumachita nkhondo...Yak 4:2zimene zimachita nkhondo...1 Pet 2:11kudabuka nkhondo kumwamba...Chiv 12:7nachita nkhondo molungama...Chiv 19:11

NKHONDO (wars)ndi pomenya nkhondo...Mas 46:9phokoso la nkhondo...Mat 24:6zikhumbitso zanu zochita nkhondo...Yak 4:1

NKHOPE (countenance)Yehova akweze nkhope yake...Num 6:26sanagwetsa kusangalala kwa nkhope...Yob 29:24kuunika kwa nkhope yanu...Mas 4:6musakhale ndi nkhope yachisoni...Mat 6:16kuyang’anitsa pankhope ya Mose...2 Akor 3:7nkhope yake ngati dzuwa...Chiv 1:16[onaninso: kuoneka, maonekedwe]

NKHOPE (face)Mulungu nkhope ndi nkhope...Gen 32:30khungu la nkhope yake...Eks 34:29anaika chophimba pa nkhope yake ...Eks 34:33Yehova awalitse nkhope yake...Num 6:25anatembenuzira nkhope yake kukhoma...2 Maf 20:2mwana pankhope panu...Yob 1:11ndidzapenyerera nkhope yanu...Mas 17:15mubisiranji nkhope yanu...Mas 44:24atiwalitsire nkhope yake...Mas 67:1iwalitsa nkhope yake...Mlal 8:1machimo anu abisa nkhope...Yes 59:2ndakhwimitsa nkhope yako...Ezek 3:8manyazi a nkhope yathu...Dan 9:7mthenga wanga pankhope...Mat 11:10nkhope yake inawala...Mat 17:2ulemelero wa nkhope yake...2 Akor 3:7ndi nkhope yosaphimbika...2 Akor 3:18wakuyang’anira nkhope yake...Yak 1:23

Page 116: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

nkhope ya Ambuye ili pa...1 Pet 3:12nadzaona nkhope yake...Chiv 22:4[onaninso: maso]

NKHOPE (faces)pankhope pawo sipadzachita manyazi...Mas 34:5obisira anthu nkhope zao...Yes 53:3usaope nkhope zao...Yer 1:8ndi nkhope zao zotumbulika...Yer 30:6musakhale ndi nkhope zachisoni...Mat 6:16

NKHOPE (presence)nkhope yanga idzamuka nawe...Eks 33:14musamaopa nkhope ya munthu...Deut 1:17pankhope panu pali chimwemwe...Mas 16:11[onaninso: pamaso]

NKHOSA YAMPHONGO (ram)ndidaona nkhosa yamphongo...Dan 8:3nsembe za nkhosa zamphongo...Mas 66:15nkhosa zamphongo za ku...Yes 60:7

NKHOSA (flock)wakusogolera Yosefe ngati nkhosa...Mas 80:1koma simudyetsa nkhosa...Ezek 34:3inu nkhosa zanga, nkhosa...Ezek 34:31zidzabalalika nkhosa za...Mat 26:31nkhosa zina ndili nazo...Yoh 10:16[onaninso: gulu, gulu la nkhosa, zoweta]

NKHOSA (sheep)ndasokera ngati nkhosa...Mas 119:176monga momwe nkhosa...Yes 53:7ngati nkhosa zokaphedwa...Yer 12:3anali ngati nkhosa...Yer 50:6tsopano nkhosa zangazo...Ezek 34:11nkhosa zamphongo ndi atonde...Ezek 34:17ndi nkhosa zidzabalalika...Zek 13:7ndikutumizani inu monga nkhosa...Mat 10:16nadzakhalitsa nkhosa ndi dzanja...Mat 25:33munthu ndani wa inu ali nazo nkhosa...Luk 15:4ndi nkhosa zimva mau ake...Yoh 10:3ndipo sasamala nkhosa...Yoh 10:13ndipo nkhosa zina ndili nazo...Yoh 10:16ngati nkhosa anatengedwa...Mac 8:32munali kusochera ngati nkhosa...1 Pet 2:25

NKHOSWE (advocate)tili nayo nkhoswe...1 Yoh 2:1

NKHOSWE (helper)adzakupatsani inu nkhoswe...Yoh 14:16pamene wafika nkhoswe...Yoh 15:26[onaninso: mthandizi]

NKHOSWE (mediator)nkhoswe ya pangano labwino...Aheb 8:6nkhoswe ya chipangano chatsopano...Aheb 12:24[onaninso: mkhalapakati]

NKHUNDA (dove)nkhundayo idabwerera...Gen 8:9ndinkabuula ngati nkhunda...Yes 38:14Aefuremu ali ngati nkhunda...Hos 7:11akutsika ngati nkhunda...Mat 3:16[onaninso: njiwa]

NKHUNDA (doves)modandaula ngati nkhunda...Yes 59:11ndi ofatsa ngati nkhunda...Mat 10:16mipando ya ogulitsa nkhunda...Mat 21:12

NKHUNI (fuel)

anthunso ali ngati nkhuni...Yes 9:19auponya kumoto kuuyesa nkhuni...Ezek 15:4

NKHUYU (figs)mitanga iwiri ya nkhuyu...Yer 24:1kapena nkhuyu pa nthula...Mat 7:16kapena mpesa kubala nkhuyu...Yak 3:12samatchera nkhuyu paminga...Luk 6:44[onaninso: mikuyu]

NKHWANGWA (axe)nkhwangwa nkuguluka...Deut 19:5adatenga nkhwangwa...Ower 9:48nkhwangwa yake idaguluka...2 Maf 6:5nkhwangwa ikakhala yobuntha...Mlal 10:10kodi nkhwangwa ingathe...Yes 10:15pali pano nkhwangwa...Mat 3:10

NOBU (Nob)mzinda wa ansembe; Davide anathawirako...1 Sam 21:1-9ansembe ochokera kumeneku, anaphedwa ndi Saulo...1 Sam22:9-23

NODI (Nod)malO (kummwera kwa Edeni) a ukapolo wa Kaini...Gen4:16,17

NOWA (Noah)mwana wa Lameki...Gen 5:28-32anapeza chisomo ndi Mulungu; anatumidwa kumangachombo/chingalawa...Gen 6:8-22analowa mchombo ndi kupulumuka pa chigumula...Gen 7anatuluka mchombo, namanga guwa la nsembe, analandiralonjezo la Mulungu...Gen 8pangano la Mulungu ndi iye...Gen 9:1-7anadalitsa ndi kutemberera ana ake; anafa...Gen 9:18-29

NSAKALI ZA MOTO (firebrands)anangoponya nsakali za moto...Miy 26:18[onaninso: miuni]

NSALU (cloth)chigamba cha nsalu yatsopano...Mat 9:16naukulunga m’nsalu yoyera...Mat 27:59mwana wakhanda wokuta ndi nsalu...Luk 2:12anaona nsalu zabafuta zitakhala...Yoh 20:5

NSANJE (envy)nsanje imakantha opanda...Yob 5:2nsanje munthu wa chiwawa...Miy 3:31nsanje imaoletsa mafupa...Miy 14:30usamachita nsanje ndi anthu ochimwa...Miy 23:17chidani chao ndi nsanje yao...Mlal 9:6[onaninso: kaduka, njiru]

NSANJE (zeal)adzautsa nsanje ngati munthu wankhondo...Yes 42:13Ziyoni ndi nsanje yaikulu ndipo ndimchitira...Zek 8:2[onaninso: changu]

NSAUKO (affliction)pothawira panga tsiku la nsauko...Yer 16:19Taonani Yehova nsauko wanga...Mali 1:9[onaninso: chisautso, kuthyoka, kuzunza, kuzunzika, masautso,mazunzo, nthenda]

NSAUKO (distress)mukakhala nao nsauko...Deut 4:30[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, nsautso, opsa,

psinjika, saukira, sautsika]

NSAUTSO (distress)

Page 117: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

anapulumutsa moyo wanga m’nsautso...1 Maf 1:29inu vuto ndi nsautso...Miy 1:27[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, opsa, psinjika,saukira, sautsika]

NSEMBE (offering)moyo wake ukapereka nsembe yopalamula...Yes 53:10nadzipereka yekha m’malo mwathu chopereka ndi nsembe...Aef5:2komatu ngatinso ndithiridwa pa nsembe...Afil 2:17[onaninso: chopereka, zopereka]

NSEMBE (offerings)napereka nsembe zopsereza paguwapo...Gen 8:20nsembe zopsereza zamphumphu ndi za kwa...Aheb 10:6[onaninso: zopereka]

NSEMBE (sacrifice)anazipha napereka nsembe...Gen 8:20ukunyoza nsembe zanga...1 Sam 2:29simudafune nsembe...Mas 40:6ndidzapereka kwa inu nsembe...Mas 116:17koposa kupereka nsembe...Miy 21:3ali ndi nsembe mu mzinda...Yes 34:6nsembe zothokozera Mulungu...Yer 33:11amapereka nsembe za nyama...Hos 8:13ine ndidzapereka nsembe...Yon 2:9adzaperekedwe ngati nsembe...Zef 1:7mukaperekera nsembe nyama...Malak 1:8osati nsembe ai...Mat 9:13monga nsembe imayeretsedwa...Marko 9:49nsembe ya fungo lokondweretsa...Aef 5:2nsembe imene Mulungu...Afil 4:18pakudzipereka yekha nsembe...Aheb 9:26khristu adapereka nsembe...Aheb 10:12palibenso nsembe ina... Aheb 10:26kwa Mulungu nsembe...Aheb 11:4Mulungu ngati nsembe...Aheb 13:15ngati otsiridwa pa nsembe...Afil 2:17mwa ansembe imodzi yomweyo...Aheb 10:14sipafunikanso nsembe...Aheb 10:18

NSEMBE (sacrifices)nsembe imene Mulungu...Mas 51:17nsembe zanu zochuluka...Yes 1 :11nsembe zanu zachabechabe...Yes 1:13yamphongo ngati nsembe...Yes 66:3nsembe zao sizindikondweretsa...Yer 6:20nsembe zimene zinkaperekedwa...Dan 8:11kupereka nsembe zopsereza...Marko 12:23adzipereka nsembe poyamba...Aheb 7:27nsembe zotere zimakondweretsa Mulungu...Aheb 13:16nsembe zochokera kumtima...1 Pet 2:5

NSENGA (dregs)wakhala pansenga...Yer 48:11[onaninso: ndungundungu]

NSINGA (chains)osanena nzinga izi...Mac 26:29[onaninso: maunyolo, ndende, nkhata, zomangira]

NSOMBA (fish)monga nsomba zigwidwira...Mlal 9:12Chauta adatuma chinsomba...Yon 1:17kuti azikhala ngati nsomba...Hab 1:14kapena atapempha nsomba...Mat 7:10anali m’mimba mwa chinsomba...Mat 12:40msanu yekha ndi nsomba zisanu...Mat 14:17adateronso ndi nsomba zija...Yoh 21:13

NSWALA (deer)

Nafitali ndi nswala...Gen 49:21monga nswala ipuma wefuwefu...Mas 42:1wopunduka adzatumpha ngati nswala...Yes 35:6

NTCHENTCHE (flies)mitambo ya ntchentche...Mas 78:45ntchentche zakufa zinunkhitsa...Mlal 10:1[onaninso: mizaza]

NTCHENTCHE (swarms)adawatumizira miambo ya ntchentche...Mas 78:45ntchenthe zakufa zimaika...Mlal 10:1

NTCHITO (business)akuchita ntchito zawo...Mas 107:23[onaninso: malonda]

NTCHITO (act)anapenya ntchito...Deut 11:7Yehova achite...Mas 119:126ntchito yake...Yes 28:21mkati mochita...Yoh 8:4

NTCHITO (actions)amaweruza ntchito...1 Sam 2:3zolungama anazichita...Owe 5:11udzalemekezera ntchito...Mas 145:4mphamvu za ntchito...Mas 145:4

NTCHITO (deeds)lalikirani mwa anthu ntchito...Mas 9:11chilango pazochita zao...Mas 99:8anaziipsa nazo ntchito zao...Mas 106:39apitiriza kuchita zoipa..Yer 5:28pakuti ntchito zao zinali zoipa...Yoh 3:19muchita ntchito za atate wanu...Yoh 8:41kolingana ndi ntchito zake...Aro 2:6mufetsa zochita zake za...Aro 8:13ayanjana nazo ntchito zake zoipa...2 Yoh 11[onaninso: machitidwe]

NTCHITO (work)Mulungu adamaliza ntchito...Gen 2:2Mose adamaliza ntchito...Eks 40:33adaikapo mtima pa ntchitoyo...Neh 4:6ntchito ya manja anu...Yob 14:15onsewo ndiwo ntchito yamanja...Yob 34:19ntchito ya zala zanu...Mas 8:3zakumwamba ndizo ntchito ya manja...Mas 102:25amapita ku ntchito yake...Mas 104:23ntchito zake ndi za ulemu...Mas 111:3ntchito zonse za Mulungu...Mlal 8:17ukupitako kulibe ntchito...Mlal 9:10adatsiriza ntchito yake...Yes 28:21ife tonse tili ntchito ya manja anu...Yes 64:8pogwiritsa ntchito anthu...Yer 22:13makhalidwe ake ndi ntchito...Yer 32:19pakuti ndichita ntchito masiku anu...Hab 1:5pita ukagwire ntchito...Mat 21:28kuti tichite ntchito za Mulungu...Yoh 6:28ntchito ya Mulungu ndi iyi...Yoh 6:29tigwire ntchito za Atate...Yoh 9:4pakutsiriza ntchito imene...Yoh 17:4sikulinso ndi ntchito ai...Aro 11:6chisakuwonongetseni ntchito...Aro 14:20ntchito za munthu...1 Akor 3:13zipatso za ntchito yanga...1 Akor 9:1gwirani ntchito ya Ambuye...1 Akor 15:58chanu mwa ntchito zanu...1 Ates 1:3wosafuna kugwira ntchito...2 Ates 3:10amawagwiritsa ntchito...Yak 1:25

Page 118: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: chita, chitira]

NTCHITO (worked)aja ankagwira ntchito...Neh 4:17Mulungu adaigwiritsa ntchito...Aef 1:20Ambuye ankagwira nawo ntchito...Marko 16:20akugwira ntchito mpaka tsopano...Yoh 5:17ikugwira ntchito mwa ife...Aef 1:19anthu akamzigwiritsa ntchito...Akol 2:22amenewa sagwira ntchito...2 Ates 3:11[onaninso: chita]

NTCHITO (works)muganizire ntchito zodabwitsa...Yob 37:14ntchito zake nzodabwitsa...Mas 66:5ntchito zanu sikukula kwake...Mas 92:5ntchito zanu nzambiri...Mas 104:24ntchito za Chauta nzazikulu...Mas 111:2ntchito zake sizimpatsa...Miy 31:31ndikudziwa ntchito zao...Yes 66:18adzamuonetsa ntchito zoposa...Yoh 5:20ntchito zimene ine ndimachita...Yoh 10:25ntchito zimene ndimachita Ine...Yoh 14:12cha ntchito za munthu...Aro 9:11tileke ntchito za mdima...Aro 13:12amene amagwiritsa ntchito...1 Akor 12:6pakuchita ntchito zolamulidwa...Agal 2:16umene ukugwira ntchito...Aef 2:2sapulumuka chifukwa cha ntchito...Aef 2:9amagwira ntchito mwa inu...Afil 2:13anthu ake achangu pa ntchito...Tit 2:14kusiya ntchito zosapindulitsa...Aheb 6:1

NTHAKA (ground)nthaka ikhale yotembereredwa...Gen 3:17nthaka idzapatsa zobala zake...Zek 8:12zinagwa pa nthaka yabwino...Mat 13:8[onaninso: malo, munda]

NTHAMBI (boughs)ndi nthambi zake zakunga...Mas 80:10[onaninso: mphanda]

NTHAMBI (branch)pakuti nthambi yake siidzaphukira...Yob 15:32nthambi ya kanjeza...Yes 9:14ndi nthambi yoturuka...Yes 11:1Davide nthambi yoongoka...Yer 23:5nthambi yolungama kuchokera kwa Davide...Yer 33:15wotchedwa dzina loti nthambi...Zek 3:8munthu wotchedwa nthambi...Zek 6:12nthambi zake zayamba...Mat 24:32amadula nthambi iliyonse...Yoh 15:2nthambi siingathe kubala zipatso...Yoh 15:4monga nthambi yodulidwa...Yoh 15:6[onaninso: mphanda]

NTHAMBI (branches)nthambi zake zimatambalala...Yob 8:16udzaphukadi nthambi ngati...Yob 14:9ndipo adzasadza nthambi...Yes 18:5ndipo nthambi zake zidzapserera...Yer 11:16nthambi zake zidzatambalala...Hos 14:6inu ndinu nthambi...Yoh 15:5ngati nthambi zina zinathyoledwa...Aro 11:17

NTHAMBO (pangs)nthambo za imfa...Mas 18:4[onaninso: zowawa]

NTHANO ZOPEKA (fables)mtima pa nthano zopeka...1 Tim 1:4

ndipo adzangotsata nthano chabe...2 Tim 1:4sitidatsate nthano zongopeka...2 Pet 1:16

NTHANTHI (by word)andiyesanso nthanthi...1 Maf 9:7

NTHAWI (ages)chitsirizo cha nthawizo...Aheb 9:26[onaninso: mibadwo, nyengo]

NTHAWI ZONSE (forever)tiyenera kuwamvera nthawi zonse...Deut 29:29kukhala moyo nthawi zonse...Yob 7:16tichinjirizeni nthawi zonse...Mas 12:7malonjezo ake nthawi zonse...Mas 146:6kumtamanda nthawi zonse...2 Akor 11:31[onaninso: muyaya]

NTHAWI ZONSE (continually)ndidzayamika Chauta nthawi zonse...Mas 34:1[onaninso: kosalekeza]

NTHAWI ZONSE (always)pamaso pake nthawi zonse...Miy 8:30simuli ndi ine nthawi zonse...Mat 26:11pakuti nthawi zonse muli nawo...Mat 26:11ndili nanu masiku onse...Mat 28:20iwe uli ndi ine nthawi zonse...Luk 15:31kupemphera nthawi zonse...Luk 18:1ntchito ya Ambuye nthawi zonse...1 Akor 15:58mwa Ambuye nthawi zonse...Afil 4:4tidzakhala ndi Ambuye nthawi zonse...1Ates 4:17okonzeka nthawi zonse...1 Pet 3:15

NTHENDA (affliction)ndi chabe ndi nthenda yoipa...Mlal 6:2[onaninso: chisautso, kuthyoka, kuzunza, kuzunzika, masautso,mazunzo, nsauko]

NYADA (boast)kuwopa kuti angamanyade...Aef 2:9musamanyada ndi kutsutsana...Yak 3:14odzikuza ndi onyada...Aro 1:30okonda ndalama, onyada...2 Tim 3:2[onaninso: kuza, nyadira]

NYADA (boastful)anthu onyada sangathe kuonekera...Mas 5:5pamenepa munthu onganyadenso...Aro 3:27mumanyada ndi kudzitama...Yak 4:16[onaninso: kuza, nyadira]

NYADA (proud)nyumba ya munthu wonyada...Miy 15:25yense wonyada mtima...Miy 16:5wabalalitsa anthu a mtima wonyada...Luk 1:51[onaninso: dukidwa, kudzikuza, kudzitama]

NYADIRA (boast)moyo wanga umanyadira Chauta...Mas 34:2takhala tikunyadira mphamvu...Mas 44:8ndipo umanyadira Mulungu...Aro 2:17mudzatha kutinyadira ife...2 Akor 1:14osanyadira ntchito imene...2 Akor 10:16kuti inenso ndinyadirepo...2 Akor 11:16[onaninso: kuza, nyada]

NYADIRA (boastful)andichotsere chifukwa chimene ndikunyadira...1 Akor 9:15ndipo ndimakunyadirani...2 Akor 7:4munthu wonyadira mphatso...Miy 25:14[onaninso: kuza, nyada]

Page 119: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

NYADIRA (pride)ankanyadira chuma chake...Ezek 16:49ana a Yakobo amanyadira...Amo 8:7kunyadira za moyo uno...1 Yoh 2:16[onaninso: kudzikuza, kudzitama, kudzitukumula, kunyada]

NYALANYAZA (careless)wonyalanyaza mayendedwe ake...Miy. 19:16)

NYALUGWE (leopard)nyalugwe adzagona pansi ndi...Yes 11:6kapena nyalugwe maanga ake...Yer. 13:23

NYAMA (animal)nyama zonse zodyedwa...Gen 7:2munthu akakantha nyama...Lev 24:18anamuika iye pa nyama pake...Luk 10:34

NYAMA (animals)ndi zinyama monga mwa mitundu...Gen 6:20za nyama zonenepa...Mas 66:15mmenemo munali nyama...Mac 10:12ngati mbalame ndi nyama...Aro 1:23

NYAMA (beast)musunga munthu ndi nyama...Mas 36:6ndinali ngati nyama...Mas 73:22amapereka chakudya kwa nyama...Mas 147:9ingakhale nyama ikakhudza...Aheb 12:20[onaninso: chirombo]

NYAMA (beasts)tiyesedwa bwanji ngati nyama...Yob 18:3afanana ndi nyama zakuthengo...Mas 49:12[onaninso: zamoyo, zirombo]

NYAMBITA (devouring)ndi lawi la moto wonyambita...Yes 29:6[onaninso: ononga]

NYAMA (meat)kapena kutipezera nyama...Mas 78:20adawagwetsera nyama yochuluka...Mas 78:27nkwabwino kusadya nyama...Aro 14:21sidzadya konse nyama...1 Akor 8:13mungathe kudya nyama iliyonse...1 Akor 10:25

NYAMUKA (arise)nyamuka, wala...Yes 60:1ndidzanyamuka ndipite...Luk 15:18[onaninso: tuluka, uka]

NYAMULA (bear)kuti anyamule mtanda wake...Marko 15:21tiyenera kunyamula zofooka...Aro 15:1nyamuliranani zothodwetsa...Agal 6:2[onaninso: bala]

NYAMULA (bore)koma ananyamula machimo a ambiri...Yes 53:12nanyamula nthenda zathu...Mat 8:17[onaninso: bala, bereka, senza]

NYAMULA (carried)anakunyamulani monga anyamula...Deut 1:31zoonadi Iye ananyamula zowawa...Yes 53:4[onaninso: tenga]

NYAMULA (carry)Mulungu wanu anakunyamulani...Deut 1:31

ananyamula zowawa zathu...Yes 53:4sindiyenera kunyamula...Mat 3:11[onaninso: senza, tenga]

NYANJA YAMCHERE (Salt Sea)Pamenepo ndi pa Nyanja ya mchere...Gen 14:3kuchidikha ndiyo Nyanja ya mchere...Deut 3:17Malekezero a Nyanja ya mchere...Num 34:3kudzakhala ku Nyanja ya mchere...Num 34:12

NYANJA YA MEDITERENIYANI (Mediterranean Sea)inalongosoledwa ngati:nyanja...Gen 19:13nyanja yayikulu...Yos 1:4;9:1nyanja ya Afilisti...Eks 23:31nyanja ya kuzambwe...Deut 11:24;Yosw 2:20; Zek 14:8

NYANJA (sea)amphamvu m’nyanja...Eks 15:4kuli nyanja yaikulu...Mas 104:25adakayenda kunyanja...Mas 107:23ankaika malire a nyanja...Miy 8:29nyanja yaikulu itha...Yes 50:2madzi amadzadzira nyanja...Hab 2:14mphepo ndi nyanja yomwe...Mat 8:27ngati nyanja yagalasi yonyezimira...Chiv 4:6pamphepete pa nyanja...Chiv 15:2ndipo nyanja panalibenso...Chiv 21:1

NYANSA (abhor)nchifukwa chake ndekha ndizinyansa...Yob 42:6[onaninso: dana, ipidwa, nyansidwa]

NYANSA (abominable)musamadzinyansitsa...Lev 11:43wochita ntchito zonyansa...Mas 14:1ngati nthambi yonyansa...Yes 14:19musachitetu chonyansa...Yer 44:4popeza ali onyansidwa...Tit 1:16m’kukhumba zonyansa...1 Pet 4:3ndi onyansa...Chiv 21:8

NYANSA (abomination)abusa onse anyansira...Gen 46:34Mulungu wathu chonyansa...Eks 8:26ndiwakhalire chonyansa...Mas 88:8zisanu ndi ziwiri nzinyansi...Miy 6:6zoipa zinyansa...Miy 8:7muyeso wonyenga unyansa...Miy 11:1wonyoza anyansa...Miy 24:9pemphero lake linyansa...Miy 28:9munthu woipa anyansa...Miy 29:27nsembe zofukiza zindinyansa...Yes 1:13nadzaimitsa chonyansa...Dan 11:31nichidzaimirira chonyansa...Dan 12:11mukadzaona chonyansa...Mat 24:15chiri chonyansa...Luk 16:15

NYANSA (abominations)zonyansa za amitundu aja...Deut 18:9ukondwerera m’zonyansa...Yes 66:3udzachotsa chonyansa...Yer 4:1ndaona zonyansa...Yer 13:27zonyansa zazikulu...Ezek 8:6kuti achite zonyansa….Ezek 8:17ataye zonyansa...Ezek 20:7uudziwitse tsono zonyansa...Ezek 22:2chagolide chodzala ndi zonyansa...Chiv 17:4wachigololo wa zonyansitsa...Chiv 17:5

NYANSA (loathe)

Page 120: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndinyansidwa nao moyo wanga...Yob 7:16onyansa pamaso pao pa iwo eni...Ezek 6:9koma oipa anyansa...Miy 13:5

NYANSIDWA (abhor)ndikunyansidwa ndi zimene ana a...Amo 6:8[onaninso: dana, ipidwa, nyansa]

NYANSIDWA (abhorred)adanyansidwa nawo anthu akewo...Mas. 106:40

NYANSIDWA (abhorrence)anthu amitundu yonse poona adanyansidwa nawo...Yes 66:24

NYANSIDWA (abhors)moyo wako umanyansidwa ndi chakudya...Yob 33:20

NYANSITSA (abhorrent)mwatinyansitsa pamaso pa Farao...Eks 5:21

NYAZITSA (despise)mufuna kunyazitsa mpingo...1 Akor 11:22[onaninso: nyoza, peputsa]

NYAZITSA (insult)chipongwe, ankanyazitsa ndi...Luk 18:32[onaninso: nyozeka]

NYEKA (consuming)anali ngati moto wonyeketsa...Eks 24:17pamaso panu ngati moto wonyeketsa...Deut 9:3Mulungu wathu ndiye moto wonyeketsa...Aheb 12:29

NYEKA (consumed)chirikuyaka moto koma osanyeka...Eks 3:2[onaninso: itha, ononga, tentha]

NYEMA (break)m’kunyema mkate ndi mapemphero...Mac. 2:42ndipo ananyema mkate...Mac 2:46posankhana ife kunyema mkate...Mac. 20:7[onaninso: phwanya]

NYEMA (broke)anadalitsa, nanyema...Mat 14:19ananyema, nati...1 Akor 11:24[onaninso: iswa]

NYENGA (cheat)koma muipsa nimunyenga...1 Akor 6:7aliyense asakunyengeni ndi kulanda...Akol 2:18[onaninso: kulanda, sautsa]

NYENGA (deceive)Yehova atero, musadzinyenge...Yer 37:9kotero kuti akanyenge...Mat 24:24munthu asadzinyenge yekha...1 Akor 3:18asakunyengeni munthu ndi mau...Aef 5:6tilibe uchimo, tidzinyenga tokha...1 Yoh 1:8njoka idandinyenga ine...Gen 3:13mtima wodzinyenga wampambutsa...Yes 44:20mwa lamulo udandinyenga ine...Aro 7:11monga njoka idanyenga Heva...2 Akor 11:3koma mkazi ponyengedwa...1 Tim 2:14nalingilira zonyenga tsiku lonse...Mas 38:12ndi mau onyenga...2 Pet 2:3nanyenge mbale wake...1 Ates 4:6

NYENGERERA (allure)anyengerera pa zilakolako za thupi...2 Pet 2:18[onaninso: kopa]

NYENGERERA (Beguiling)kunyengerera iwo amoyo...2 Pet 2:14

NYENGO YACHISANU (winter)padzakhala nyengo yachisanu...Gen 8:22

NYENGO (ages)pasanakhale nyengo zapansi...1 Akor 2:7[onaninso: mibadwo, nthawi]

NYENYESWA (crust)udzamaliza ndi nyenyeswa...Miy 6:26

NYERERE (ant)pita kwa nyerere...Miy 6:6

NYEZIMIRITSA (adorn)wake anyezimiritsa...Yob 26:13[onaninso: kometsedwa, kometsera, kongoletsa]

NYIMBO (melody)uimbenso nyimbo zake...Yes 23:16Masalimo ndi a nyimbo...Aef 5:19

NYONGA (power)chifukwa cha nyonga zanu...Eks 15:6nyonga ndi mphamvu zake...Yes 40:26ulemerero ndi nyonga...Chiv 5:13[onaninso: mphamvu]

NYOZA (blaspheme)kodi mdani adzanyoza...Mas 74:10[onaninso: mwano]

NYOZA (blasphemed)anthu opusa ananyoza dzina...Mas 74:18[onaninso: mwano, tonzedwa]

NYOZA (despise)mukamanyoza malamulo anga...Lev 26:15anthu ondinyoza inenso...1 Sam 2:30usamanyoza amai ako atakalamba...Miy 23:22ndimadana nawo ndipo ndimawanyoza...Amo 5:21ansembe inu amene mumanyoza...Mal 1:6kwa m’modzi, nkumanyoza winayo...Mat 6:24namanyoza ulamuliro...2 Pet 2:10[onaninso: nyazitsa, peputsa]

NYOZA (despised)adanyoza mau a woyera uja...Yes 5:24anthu adamnyoza ndipo adamkana...Yes 53:3zonyozeka zidzakhala zenizeni...1 Akor 1:28

NYOZA (despises)wonyoza malangizo amadziononga...Miy 13:13amene amanyoza mnzake ngwochimwa...Miy 14:21mwana wopusa amanyoza amai ake...Miy 15:20anthu anga anyoza ndodo yanga...Ezek 21:10adawanyoza manyazi a imfa...Aheb 12:2[onaninso: peputsa]

NYOZA (dishonours)anyoza mutu wake...1 Akor 11:4[onaninso: peputsa]

NYOZA (reject)adzaleka liti kundinyoza...Num 14:11[onaninso: kaniza, pepula, nyoza]

NYOZEKA (base)ndi onyozeka pa olemekezedwa...Yes 3:5ndi zonyozeka...1 Akor 1:28

Page 121: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

NYOZEKA (contemptible)munena, gome la Yehova nlonyozeka...Mal 1:7ndakuikani onyozeka...Mal 2:9[onaninso: achabe]

NYOZEKA (insult)musanyengedwe, Mulungu sanyozeka...Agal 6:7[onaninso: nyazitsa, nyoza]

NYOZERA (neglect)usanyozere mphatso yaulele...1 Tim 4:14

NYUMBA YANTCHITO (booth)ali pantchito nyumba ya...Mat 9:9

NYUMBA ZACHIFUMU (palaces)nyumba zanu zachifumu...Mas 45:8Mulungu adziwika mzinyumba zake...Mas 48:3ngakhale mnyumba zathu zaufumu...Yer 9:21

NYUMBA YA MFUMU (palace)polowa mnyumba ya mfumu...Mas 45:15nyumba ya alendo kuti isakhale...Yes 25:2olonda nyumba ya mfumu...Afil 1:13

NYUMBA (building)ndinunso nyumba ya Mulungu...1 Akor 3:9nyumba ina imene Mulungu...2 Akor 5:1mwa iyeyu nyumba yonse...Aef 2:21[onaninso: mangirira]

NYUMBA (house)ndi kunyumba ya atae wako...Gen 12:1koma ine ndi a m’nyumba yanga...Yos 24:15ndi kunyumba yokomanamo...Yob 30:23ndinawatsogolera kunyumba ya Mulungu...Mas 42:4zokoma za m’nyumba yanu...Mas 65:4nyumba yake itsikira kuimfa...Miy 2:18nzeru imangitsa nyumba...Miy 24:3kunka kunyumba ya maliro...Mlal 7:2omwe asunga nyumba adzathunthumira...Mlal 12:3ku nyumba ya Mulungu ya Yakobo...Yes 2:3aphatikiza nyumba ndi nyumba...Yes 5:8nyumba inadzazidwa ndi utsi...Yes 6:4konza nyumba yako...Yes 38:1kuwasangalatsa m’nyumba yanga...Yes 56:7zinagunda pa nyumbayo...Mat 7:25nyumba yanga idzanenedwa nyumba...Mat 21:13kuti nyumba yanga idzale...Luk 14:23musamayesa nyumba ya Atate anga...Yoh 2:16M’nyumba ya Atate wanga alimo...Yoh 14:2pabwalo ndi m’nyumba m’nyumba...Mac 20:20zaka ziwiri zamphumphu m’nyumba yake...Mac 28:30woweruza bwino nyumba yake...1 Tim 3:4mpingo uli m’nyumba yako...Fil 2pakuti nyumba iriyonse...Aheb 3:4wosunga nyumba yake ndife nyumba...Aheb 3:6musamlandire iye kunyumba...2 Yoh 1:10[onaninso: banja]

NYUMBA (household)ngati nyumbayo iri yoyenera...Mat 10:13[onaninso: banja]

NYUMBA (houses)nyumba zao sizitekeseka...Yob 21:9adadzadza nyumba zao ndi zabwino...Yob 22:18ayesa kuti nyumba zao zikhala...Mas 49:11nyumba ndi chuma ndizo cholowa...Miy 19:14ndipo onse amene adasiya nyumba...Mat 19:29nanga mulibe nyumba zakudyeramo...1 Akor 11:22

NYUNDO (hammer)mau anga ali ngati nyundo...Yer 23:29anali ngati nyundo ya dziko...Yer 50:23

NZERU (ability)molingana ndi nzeru zake...Mat 25:15[onaninso: kukhoza, kutha, mphamvu]

NZERU (understand)kuti aone ngati aliko anzeru...Mas 14:2amene ali anzeru pakati pa...Dan 11:33[onaninso: dziwa, dziwitsa, mvera, mvetsetsa, zindikira]

NZERU (understanding)nzeru yake njosatha...Mas 147:5nimuyende m’njira ya nzeru...Miy 9:6nzeru ndi kasupe wa moyo...Miy 16:22nzeru zake sizisanthulika...Yes 40:28[onaninso: chidziwitso, chizindikiritso, kumvera, kuzindikira,luntha, luso, mvetsa,]

NZERU (wisdom)ndinu anthu anzeru...Deut 4:6nzeru zanu zidzafera...Yob 12:2choncho muziphunzitse nzeru...Mas 51:6amene wapeza nzeru...Miy 3:13ukhale ndi nzeru...Miy 4:7ndiye chiyambi cha nzeru...Miy 9:10kupata nzeru kupambana...Miy 16:16amene amakonda nzeru...Miy 19:8nzeru ndiyapatali kwambiri...Miy 24:7nzeru zambiri zimadzetsa...Mlal 1:18ndikuti nzeru nzabwino...Mlal 9:16cha nzeru za Mulungu...Mat 11:19anakula m’nzeru...Luk 2:52nzeru zake ndi kudziwa...Aro 11:33si mu nzeru ya anthu...1 Akor 1:17Agriki amafunafuna nzeru...1 Akor 1:22nzeru za anthu odalira...1 Akor 3:19si m’nzeru ya thupi...2 Akor 1:12adziwe nzeru za Mulungu...Aef 3:10ndiye kuti nzeru ndi...Akol 2:3akunja azikhala a nzeru...Akol 4:5wa inu akasowa nzeru...Yak 1:5kulandira mphamvu, chuma, nzeru...Chiv 5:12matamando, ulemelero, nzeru...Chiv 7:12

NZERU (wise)wanzeru ndi womvetsa...Deut 4:6Mulungu ndi wanzeru...Yob 9:4anthu kuti akhale anzeru...Yob 32:9mudzakhala ndi nzeru liti...Mas 94:8munthu aliyense wanzeru...Mas 107:43usamangodziwona ngati wanzeru...Miy 3:7wa mtima wanzeru...Miy 16:21kuti chingamadziyese chanzeru...Miy 26:5mau a anthu anzeru...Mlal 12:11ndiwo anzeru ndi wopulukira...Aro 1:14ndiye yekha wanzeru...Aro 16:27ali kuti anthu anzeru...1 Akor 1:20ndinu anzeru mwa Khristu...1 Akor 4:10monga anthu opanda nzeru...Aef 5:15amene angathe kukupatsa nzeru...2 Tim 3:15anali wanzeru kuposa anthu...1 Maf 4:31amatipatsa nzeru...Yob 35:11anu amandisandutsa wanzeru...Mas 119:98nchanzeru kupambana nzeru...1 Akor 1:25

NZIMBE (cane)sunandigulire ine nzimbe...Yes 43:24seba, ndi nzimbe...Yer 6:20

Page 122: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

O

OBADIYA (Obadiah)woyang’anira za mnyumba ya mfumu Ahabu...1 Maf 18:3-16mneneri wa Yuda...Obad 1

OBEDI-EDOMU (OBED-EDOM)mfilisti wochokera ku Gati,bokosi lachipangano linasiyidwa mnyumba mwake 2 Sam6:10-12;1 Mbir 13:13,14

OBEDI (Obed)mwana wa Bowazi ndi Rute...Rut 4:17-22

OCHIMWA (sinners)mayendedwe a anthu ochimwa...Mas 1:1amaphunzitsa ochimwa...Mas 25:8kumodzi ndi anthu ochimwa...Mas 26:9ochimwa aonongeke...Mas 104:35akakukopa ochimwa usalole...Miy 1:10ochimwa agwidwa...Yes 33:14koma anthu ochimwa...Mat 9:13amisonkho ndi ochimwa...Mat 11:19pakuti ochimwa omwe akonda...Luk 6:32analli anthu akuchimwa koposa...Luk 13:2Mulungu samvera ochimwa...Yoh 9:31pamene tinali ochimwabe...Aro 5:8ambiri anayesedwa ochimwa...Aro 5:19anthu ochimwa ndi...1 Tim 1:9adzapulumutse anthu ochimwa...1 Tim 1:15wosiyana ndi ochimwa...Aheb 7:26kwa anthu ochimwa...Aheb 12:3zimene ochimwa osapembedza...Yuda 15

OCHITA (doers)okhawo amene amachitadi...Aro 2:13khalani akuchita mau...Yak 1:22

OCHITIRA ZABWINO (benefactors)anenedwa ochitira zabwino...Luk 22:25

ODALA (blessed)odala iwo amene asunga...Mas 106:3nadzamutcha odala...Miy 31:28amitundu onse adzatcha inu odala...Mal 3:12Odala ali osauka muuzimu...Mat 5:3Odala ali achisoni...Mat 5:4Odala ali akufatsa...Mat 5:5Odala ali akumva njala...Mat 5:6Odala ali akuchitira chifundo...Mat 5:7Odala ali oyera mtima...Mat 5:8Odala ali akuchita mtendere...Mat 5:9Odala ali akuzunzidwa...Mat 5:10Odala muli inu m’mene...Mat 5:11Odala iye amene...Mat 11:6Maso anu ali odala...Mat 13:16Odala inu ngati mudzichita...Yoh 13:17Odala iwo akukhulupirira...Yoh 20:29adzakhala odala nkuchita...Yak 1:25Odala akufa akumwalira...Chiv 14:13Odala iwo amene ayitanidwa...Chiv 19:9Odala ndi woyera mtima...Chiv 20:6Odala iwo amene atsuka miinjiro...Chiv 22:14[onaninso: dala, dalitsa, dalitsidwa, dalitsika, wodala]

ODANDAULA (complainers)amenewo ndiwo odandaula...Yuda 16

ODEDI (Oded)mneneri wa ku Samariya...2 Mbir 28:9-15

ODZICHEPETSA (humble)phatikanani nao odzichepetsa...Aro 12:16koma apatsa chisomo odzichepetsa...Yak 4:6apatsa chisomo kwa odzichepetsa...1 Pet 5:5[onaninso: chepetsa, ofatsa, ozunzika, wodzichepetsa, wofatsa]

OFATSA (humble)adzawatsogolera ofatsa...Mas 25:9ofatsa adzakumva nadzakondwera...Mas 34:2Yehova agwirizitsa ofatsa...Mas 147:6[onaninso: chepetsa, odzichepetsa, ozunzika, wodzichepetsa,

wofatsa]

OFATSA (meek)nadzadzudzulira ofatsa...Yes 11:4ngodala anthu ofatsa...Mat 5:5mtima woleza ndi ofatsa...2 Akor 10:1zochita zake zofatsa...Yak 3:13

OFIRI (Ophir)wotchuka ndi golide...1 Mbir 29:4

OFURA (Ophrah)mzinda wa manase; kwao kwa Gideoni...Ower 6:11,15malo komwe Gideoni adaikidwa...Ower 8:32

OGI (Og)mfumu ya chiamori wa Basani...Deut 3:1-13anagonjetsedwa ndi kuphedwa ndi Israeli...Num 21:32-35

OGONTHA (deaf)makutu a ogontha adzatseguka...Yes 35:5ndi ogontha akumva...Mat 11:5[onaninso: gontha, gonthi]

OHOLA (Oholah)dzina la chizindikiro la Samariya...Ezek 23:4,5,36

OIMBA (singers)oimba nyimbo zapakamwa...Mas 68:25ndinali ndi ondiimbira nyimbo...Mlal 2:8

OIPA (evil)ndi maganizo oipa...Gen 6:5ali owerengeka ndi oipa...Gen 47:9oipa amagwadira abwino...Miy 14:19nayang’anira oipa ndi abwino...Miy 15:3ngati inu muli oipa...Mat 7:11[onaninso: choipa, woipa, zoipa]

OIPA (injustice)ndi anthu oipa amawatseka pakamwa...Yob 5:16[onaninso: chisalungamo]

OIPA (unfaithful)koma oipa adzalikhidwa...Miy 2:22[onaninso: osakhulupirika]

OIPA (unjust)pomwalira oipa chidikiro...Miy 11:7[onaninso: osalungama, wonyenga, wosalungama]

OIPA (wicked)anthu oipa adzazimirira...1 Sam 2:9kuwathandiza anthu oipa...2 Mbir 19:2oipa akhaliranji ndi moyo...Yob 21:7akalonga kuti ndinu oipa...Yob 34:18amalanga anthu oipa...Mas 7:11anthu oipa akodwa mumsampha...Mas 9:16anthu oipa adzapita...Mas 9:17munthu oipa amanyoza...Mas 10:13

Page 123: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

anthu oipa akunga uta...Mas 11:2anthu oipa adzazitamabe...Mas 94:3anthu oipa asakhaleponso...Mas 104:35kutali ndi anthu oipa...Mas 119:155ngati ndiri nao mayendewe oipa...Mas 139:24anthu oipa Mulungu...Miy 2:22kutali ndi anthu oipa...Miy 15:29oipawo zinthu sizidzawayendera...Mlal 8:13oipa asiye makhalidwe ao...Yes 55:7anthu oipa ali ngati nyanja...Yes 57:20oipa adzachitabe zoipa...Dan 12:10[onaninso: woipa, wonyenga, woparamula]

OKHULUPIRIRA (believers)khala chitsanzo kwa iwo okhulupirira...1 Tim 4:12popeza ali okhulupirira ndi okondedwa...1 Tim 6:2

OKONDA MULUNGU (devout)anthu ena okonda Mulungu...Mac 8:2[onaninso: opembedza, woopa Mulungu, wopembedza

Mulungu]

OKONDEDWA (beloved)apatsa okondedwa ake...Mas 127:2ali okondedwa...Aro 11:28[onaninso: wokondedwa]

OKONGOLA NDALAMA (bankers)ndalama zanga kwa okongoza ndalama...Mat 25:27

OKONGOLETSA (creditor)okongoletsa onse alekelere...Deut 15:2[onaninso: wokongoletsa]

OLAMULIRA (authorities)azimvera akulu olamulira...Aro 13:1[onaninso: ulamuliro]

OLAMULIRA (authority)koma polamulira woipa...Miy 29:2mukudziwa kuti olamulira...Mat 20:25[onaninso: mphamvu, ulamuliro]

OLANKHULA NDI MIZIMU (mediums)kwa olankhula ndi mizimu...Yes 8:19

OLENGEDWA (creature)cholengedwa chonse cha Mulungu...1 Tim 4:4[onaninso: cholengedwa, zamoyo]

OLIVI, PHIRI LA OLIVI (Olives, Mount Olives)Davide anathawirako...2 Sam 15:30uneneri wokhudza phiriri...Zek 14:4Yesu analowa mwachigonjetso kuchokera pamenepa...Mat 21:1mau auneneri anaperekedwa kuchokera pamenepa...Mat 24:3

OLIVI (Olive)laliwisi la mtengo wa olivi...Gen 8:11mtengo wauwisi wa olivi...Mas 52:8mitengo ya olivi ipande...Hab 3:17mtengo wa olivi wakuthengo...Aro 11:24

OLIZA CHITOLIRO (trumpeters)kapena la oliza chitoliro...Chiv 18:22

OLOWA NYUMBA (heirs)pomweponso olowa nyumba...Aro 8:17ndi olowa anzake a Khristu...Aro 8:17ali olowa nyumba pamodzi ndi ife...Aef 3:6ndi olowa nyumba aufumu...Yak 2:5wolowa nyumba pamodzi wa chisomo...1 Pet 3:7

OLUNGAMA (righteous)kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa...Gen

18:23olungama achiona nakondwera...Yob 22:19pakuti Yehova adziwa mayendedwe a olungama...Mas 1:6pakuti inu Yehova mudzadalitsa olungama...Mas 5:12koma Yehova achilikiza olungama...Mas 37:17Yehova akonda olungama...Mas 146:8koma mbeu ya olungama idzalanditsidwa...Miy 11:21koma pemphero la olungama...Miy 15:29koma olungama alimba mtima ngati mkango...Miy 28:1pochuluka anthu olungama anthu akondwa...Miy 29:7anthu ako adzakhalanso onse olungama...Yes 60:21sindinadza kudzaitana olungama koma ochimwa...Mat 9:13aneneri ambiri ndi anthu olungama analakalaka...Mat 13:17pomwepo olungamawo adzawalitsa monga dzuwa...Mat 13:43ndipo onse awiri anali olungama mtima...Luk 1:6mwa iwo okha kuti ali olungama...Luk 18:9maweruziro anu ali oona ndi olungama...Chiv 16:7[onaninso: chilungamo,wolungama, zolungama]

OMBA (blow)anaombetsa mmwamba mphepo...Mas 78:26muombe pamunda...Nyi 4:16mpweya wa Yehova waombapo...Yes 40:7mphepo iomba pomwe ifuna...Yoh 3:8[onaninso: chotsa]

OMBA (clap)anthu adzamuombera mmanja...Yob 27:23ombani mmanja mitundu yonse...Mas 47:1mitsinje iombe mmanja...Mas 98:8idzaomba mmanja mwao...Yes 55:12

OMBEZA (divination)musamaombeza kapena...Lev 19:26[onaninso: mlauli, kulosa, mbwebwe]

OMBOLA (atonement)iomboledwa ndi chifundo ndi ntheradi...Miy 16:6[onaninso: kuchotsedwa, kufafaniza, kuyanjanitsa, mwambowopepesera machimo]

OMBOLA (deliver)silingathe kuombola...Yes 50:2[onaninso: landitsa, pulumutsa]

OMURI (Omri)anapangidwa mfumu ya Israeli ndi ankhondo...1 Maf16:16,21,22anamanga Samariya, analamulira moipa...1 Maf 16:23-27

ONA (see)koma sungathe kuona...Eks 33:20ndidzamuwona Mulungu...Yob 19:26mudzaone zimene Mulungu...Mas 66:5kuti angaone ndi maso ao...Yes 6:10choncho adzaona zidzukulu...Yes 53:10pakuti adzaona Mulungu...Mat 5:8amapenya, komabe saona...Mat 13:13ndinakuona patsinde...Yoh 1:50anakondwera kuona tsiku langa...Yoh 8:56tifuna kuona Yesu...Yoh 12:21koma inu mudzandiona...Yoh 14:19kuti Iye akadzaoneka...1 Yoh 3:2adzidzaona nkhope yake...Chiv 22:4[onaninso: yang’ana]

ONA (behold)taona wakongolatu...Nyi 1:15onani mwana wankhosa wa Mulungu...Yoh 1:36[onaninso: onani]

Page 124: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ONA (mark)tapenya wangwiro ndipo taona woongoka mtima...Mas 37:37[onaninso: chizindikiro]

ONA (observe)pakuona mayendedwe anu ndi...1 Pet 3:2[onaninso: penyetsetsa, sunga]

ONA (seen)ndamuona Mulungu...Gen 32:30zonsezi ndidaziona...Mlal 8:9mwandionerako amene...Nyi 3:3ndani adazionapo zoterezi...Yes 66:8Taona zodabwitsa...Luk 5:26amene adaona Mulungu...Yoh 1:18maonekedwe akenso simudawaone...Yoh 5:37zimene ndidaziona...Yoh 8:38waona Ine waonanso...Yoh 14:9zimene tidaziona...Mac 4:20ndidamuona Yesu...1 Akor 4:18pa zinthu zooneka...2 Akor 4:18munthu amene anamuona...1 Tim 6:16tidamuona ndi maso...1 Yoh 1:1ndikuona anthu onse...Mas 33:13aona mnzake ali...1 Yoh 3:17akaona mbale wake...1 Yoh 5:16adzaona tsiku lakubwera...Yoh 8:56timati tidzaone Yesu...Yoh 12:21

ONAMA (liar)anthu onse ndi onama...Aro3:4sitidachimwe, tikumuyesa wonama...1 Yoh 1:10mbale wake, ndi wonama ameneyo...1 Yoh 4:20 amayesa kuti Mulungu ndi wonama...1 Yoh 5:10[onaninso: wabodza]

ONANI (behold)taonani namwali adzaima...Yes 7:14taonani Mulungu wanu...Yes 40:9taonani munthuyo...Yoh 19:5taonani chikondi cha Atate watipatsa...1 Yoh 3:1[onaninso: ona]

ONANI (Onan)mwana wachiwiri wa Yuda,anaphedwa chifukwa cholephera kupereka mbeu kwa mbalewake...Gen 38:8-10

ONDA (feeble)mnofu wanga waonda posowa...Mas 109:24[onaninso: fooka, kutha mphamvu, lefuka, onda]

ONEKA (appear)uoneke mtima...Gen 23:12amuna onse adzioneka...Deu 31:11machimo anu aoneke...Ezek 21:24adzaima ndani pooneka Iye...Malak 3:2[onaninso: onekera, onetsedwa]

ONEKA (spring)zinthu zakale zaoneka...Yes 42:9[onaninso: kasupe, meretsera, phukira]

ONEKERA POYERA (exposed)zochita zakezo zingaonekere...Yoh 3:20ndipo zonse zimaonekera poyera...Aef 5:13

ONEKERA (appear)ndikadze liti kuonekera...Mas 42:2chochita inu chionekere...Mas 90:16anaonekera mu ulemelero wake...Mas 102:16

kuti aonekere kwa anthu...Mat 6:16inunso muonekere olungama...Mat 23:28ukuti uonekere pomwepo...Luk 19:11adzaonekera panthawi yachiwiri...1 Pet 4:18ndipo anamuonekera iye mngelo...Luk 1:11amene anaonekera mu ulemelero...Luk 9:31pakuti chaonekera chisomo...Tit 2:11waonekera kuchotsa uchimo...Aheb 9:26pamene inunso mudzaonekera...Akol 3:4pakuonekera mbusa wamkulu...1 Pet 5:4kuti akaonekere...1 Yoh 2:28[onaninso: oneka, onetsedwa]

ONEKERA (manifest)ndipo moyowo unaonekera...1 Yoh 1:2[onaninso: onetsa, onetsedwa]

ONESIFOLE (Onesiphorus)mkhristu wa ku Efeso yemwe anayamikiridwa chifukwa chautumiki wake...2 Tim 1:16-18

ONESIMO (Onesimus)kapolo wa Filemoni yemwe anatembenuzidwa mtima ndi Pauloku Roma...Fil 10-17limodzi ndi Tikito, ananyamula kalata ya Paulo kupita nayo kuKolose ndi kwa Filemoni Akol 4:7-9

ONETSA (manifest)mudzionetsa nokha kwa ife...Yoh 14:22[onaninso: onekera, onetsedwa]

ONETSA (revealed)uonekera pa chisapembedzo...Aro 1:18koma anachionetsa tsopano...Akol 1:26[onaninso: onetsedwa, onetsera, ulula, vumbulutsa,

vumbulutsidwa]

ONETSEDWA (appear)tiyenera kuonetsedwa...2 Akor 5:10[onaninso: oneka, onekera]

ONETSEDWA (revealed)ulemelero umene udzaonetsedwa...Aro 8:18[onaninso: onetsa, onetsera, ulula, vumbulutsa, vumbulutsidwa]

ONETSERA (manifest)ndipo ndidzadzionetsera ndekha...Yoh 14:21ndalionetsera dzina lanu...Yoh 17:6[onaninso: oneka, onekera,onetsa]

ONETSERA (revealed)Mulungu anationetsera izi...1 Akor 2:10[onaninso: onetsa, onetsedwa, ulula, vumbulutsa,

vumbulutsidwa]

ONGOKA (equity)ndi kupotoza zoongoka zonse...Mik 3:9[onaninso: fana, lunjika, onongeka]

ONI (On)mzinda wa Ejipito wa kuzambwe, palikulu pa mapembedzedwea dzuwa...Gen 41:45,50wotchedwa Beti semesi...Yer 43:13

ONJEZA (add)musamaonjeza pa...Deut 4:2usaonjezere kanthu pa...Miy 30:6zidzaonjezedwa kwa...Mat 6:33Ambuye anawaonjezera...Mac 2:47khamu lalikulu lidaonjezedwa...Mac 11:24chinaonjezeka chifukwa cha...Agal 3:19

Page 125: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ONONGEKA (equity)ndi kuonongeka sikungalowe...Yes 59:14[onaninso: fana, lunjika, ongoka]

ONONGA (consumed)pakuti tionongeka mumkwiyo...Mas 90:7chenjerani mungaonongane...Agal 5:15[onaninso: itha, nyeka, tentha]

ONONGA (destroy)mudzaononga olungama pamodzi...Gen 18:23ndidzaononga oipa onse...Mas 101:8ndidawaononga ndi mphamvu ya...Mas 118:10Chauta adzaononga oipa onse...Mas 145:20chopweteka kapena choononga...Yes 11:9kukhululuka mtima mpaka nditawaononga...Yer 13:14ndipo muwaononge kotheratu...Yer 17:18amene akhoza kuononga moyo ndi...Mat 10:25koma kuti aononge Yesu...Mat 27:20ndidzaononga kachisi uyu...Marko 14:58kupulumutsa moyo kapena kuuononga...Luk 6:9ndidzaononga nzeru za anzeru...1 Akor 1:19Mulungu adzaononga ziwiri zonse...1 Akor 6:13akhoza kupulumutsa ndi kuononga...Yak 4:12[onaninso: pasula]

ONONGA (destruction)muwagwetsa kuti muwaononge...Mas 73:18monganso atero nao malembo ena ndi kudziononga nao eni...2

Pet 3:16[onaninso: chiwonongeko, khala fumbi, onongeka, pasula]

ONONGA (devouring)mau onse akuononga...Mas 52:4[onaninso: nyambita]

ONONGEDWA (destroyed)ndipo zinaonongedwa zamoyo...Gen 7:23ankadana nane ndidawaononga...2 Sam 22:41anthu anga aonongeka chifukwa...Hos 4:6Israeli chikuonongeka ndi ichi...Hos 13:9mumawagwetsa mpaka aonongeke...Mas 73:18aombola moyo wanga ungaonongeke...Mas 103:4akuchita zoipa adzaonongeka...Miy 10:29dziko lake silidzaonongekanso...Yes 60:18kuti lionongeke thupi...1 Akor 5:5chitsiriziro chao ndicho kuonongeka...Afil 3:19ndi kudziononga nao eni...2 Pet 3:16

ONONGEDWA (perish)ndizo zonse zakuonongedwa...Akol 2:22[onaninso: onongeka, tayika]

ONONGEKA (destruction)amene aombola moyo wako ungaonongeke...Mas 103:4koma akuchita zoipa adzaonongeka...Miy 10:29kuti lionongeke thupi...1 Akor 5:5chitsiriziro chao ndicho kuonongeka...Afil 3:19[onaninso: chiwonongeko, khala fumbi, ononga, pasula]

ONONGEKA (perish)aonongeka pakudzudzula...Mas 80:16mudzaonongeka nonse momwemo...Luk 13:3sizidzaonongeka ku nthawi yonse...Yoh 10:28chosalungama kwa iwo akuonongeka...2 Ates 2:10wosafuna kuti ena aonongeke...2 Pet 3:9[onaninso: onongedwa, tayika]

ONSE (all)anthu onse...Mlal 12:13

ONYENGA (hypocrites)pamodzi ndi anthu onyenga...Mas 26:4[onaninso: achiphamaso]

OOMBEZA (diviners)aneneri anu oombeza anu...Yer 27:9

OPA (afraid)ndipo ndinaopa chifukwa...Gen 3:10usaope, Abramu...Gen 15:1popeza anaopa...Eks 3:6wopanda wina wakukuopsani...Lev 26:6imene muwaopa...Deut 7:19sindidzaopa unyinji...Mas 3:6zopanda pake inandiopsa...Mas 18:4usaope polemezedwa...Mas 49:16tsiku la kuopa ine...Mas 56:3amaopa zizindikiro...Mas 65:8musaope monga kuopa...Yes 8:12opanda woziopsa...Yes 17:2ndani kuti uopa...Yes 51:12lakundiopsa...Dan 4:5musaope...Mat 14:27uchita choipa, opatu...Aro 13:4osaopa choopsa chiri...1 Pet 3:6

OPA (fear)ine ndimaopa Mulungu...Gen 42:18musaope anthu a m’dzikolo...Num 14:9kuti aphunzire kundiopa...Deut 4:10muzikaopa Chauta Mulungu...Deut 6:2kodi Yobu aopa Mulungu...Yob 1:9pamenepa anaopa-opatu...Mas 14:5kuopa Yehova kuli mbe...Mas 19:9sindidzaopa choipa...Mas 23:4ndidzaopai yani...Mas 27:1dziko lonse lapansi liope...Mas 33:8opani Yehova inu oyera...Mas 34:9palibe kuopa Mulungu...Mas 36:1pamenepo anaopa kwakukulu...Mas 53:5inu nonse akuopa Mulungu...Mas 66:16adzakuopani m’mene likhalira...Mas 72:5kuti aliope dzina lanu...Mas 86:11kumuopa Yehova ndiye...Mas 111:10amene akuopani adzandiona...Mas 119:74wanzeru, opa Yehova...Miy 3:7kuopa anthu kuchokera...Miy 29:25kuti anthu akaope pamaso...Mlal 3:14opa Mulungu, musunge...Mlal 12:13limbani musaope...Yes 35:4kodi simundiopa ine...Yer 5:22wosaopa inu ndani...Yer 10:7inu akuopa dzina langa...Mal 4:2musamaopa amene akupha...Mat 10:28musamaopa kagulu ka...Luk 12:32woweruza wosaopa Mulungu...Luk 18:2kodi suopa Mulungu...Luk 23:40umayenda nkuopa kwa Ambuye...Mac 9:31chifukwa cha kuopa imfa...Aheb 4:1popeza anaopa Mulungu...Aheb 5:7kondani abale, opani Mulungu...1 Pet 2:17usaope zimene uti uzamve...Chiv 2:10[onaninso: mantha]

OPA (feared)azambawo ankaopa Mulungu...Eks 1:17ngwoyenera kumuopa...1 Mbir 16:25naposa ambiri pakuopa Mulungu...Neh 7:2pamenepo iwo akuopa Yehova...Mal 3:16osaopa mkwiyo wa mfumu...Aheb 11:27[onaninso: opsa]

Page 126: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

OPA (fearing)wosaopa mkwiyo wa mfumu...Aheb 11:27[onaninso: kuopa]

OPA (fears)wakuopa Mulungu ndi kupewa...Yob 1:8munthuyo wakuopa Yehova...Mas 25:12wolumbira ndi woopa lumbiro...Mlal 9:2m’mitundu yonse wakumuopa...Mac 10:35[onaninso: mantha]

OPA (terrified)osaopa adani m’kanthu konse...Afil 1:28[onaninso: opsedwa]

OPA (terrifying)ndiopatu ndi kunthunthumira...Aheb 12:21

OPAMBANA (conquerors)pa zonsezi tili opambana...Aro 8:37

OPANDA ZIPATSO (barren)kuti musakhale aulesi kapena opanda zipatso...2 Pet 1:8[onaninso: chumba, kusabala, uma, wosaona mwana]

OPANDA CHILEMA (blameless)okondwa ndi opanda chilema...Yuda 24[onaninso: khala wosalakwa, ngwiro, panda chilema]

OPEMBEDZA MAFANO (idolaters)adama, opembedza mafano...1 Akor 6:9zaufiti, opembedza mafano...Chiv 21:8zopha anzao, zopembedza...Chiv 22:15

OPEMBEDZA (devout)ndi akupanduka opembedza...Mac 13:43[onaninso: okonda Mulungu, woopa Mulungu, wopembedzaMulungu]

OPHUNZIRA (disciple)ophunzira a Yohane Mbatizi...Mat 9:14ophunzira anu sasunga mwambo...Mat 15:2ophunzira ake khumi ndi awiri...Mat 20:17ndiye kuti ndinudi ophunzira anga...Yoh 8:31nanunso mukufuna kukhala ophunzira anga...Yoh 9:27ife ndifetu ophunzira a Mose...Yoh 9:28mumaonetsa kuti ndinu ophunzira anga...Yoh 15:8[onaninso: wophunzira]

OPSA (terrifies)Wamphamvuyonse wandiopsa...Yob 23:16

OPSA (awesome)malo ano ndi oopsa...Gen 28:17mwa iye nzoopsa zedi...Eks 34:10Mulungu wamkulu ndi woopsa...Deut 7:21Mulungu wamkulu wamphamvu ndi woopsa...Deut 10:17mthenga wa Mulungu woopsa ndithu...Ower 13:6kuchitira dziko lanu zoopsa...2 Sam 7:23Mulungu wamkulu ndi woopsa...Neh 1:5dzanja lanu lidzaphunzitsa zoopsa...Mas 45:4mudzatiyankha nazo zoopsa...Mas 65:5ntchito zanu zoopsa...Mas 66:3zochitira iye ana a anthu nzoopsa...Mas 66:5inu Mulungu ndinu woopsa...Mas 68:35akhale woopsa kwa mafumu...Mas 76:12dzina lanu lalikulu ndi loopsa...Mas 99:3adzanenera mphamvu za ntchito zanu zoopsa...Mas 145:6pamene inu muchita zoopsa...Yes 64:3

wamphamvu ndi woopsa...Yer 20:11Ambuye Mulungu wamkuru ndi woopsa...Dan 9:4

OPSA (distress)nadzawaopsa m’ukali wake...Mas 2:5[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, nsautso,psinjika, saukira, sautsika]

OPSA (feared)Inu ndinu woopsa...Mas 76:7[onaninso: opa]

OPSA (fearful)woopsa pomyamika...Eks 15:11Mulungu wamoyo nkoopsa...Aheb 10:31[onaninso: mantha]

OPSA (fearfully)nchoopsa ndi chodabwitsa...Mas 139:14

OPSA (terrify)pamenepo mundiopsa ndi maloto...Yob 7:14koma awa anadza kuziopsa...Zek 1:21[onaninso: chititsa mantha]

OPSA (terror)lochokera kwa Mulungu linandiopsa...Yob 31:23[onaninso: choopsa, kunjenjemera, mantha]

OPSEDWA (terrified)kwa inu musamaopsedwa...Deut 1:29koma anaopsedwa ndi...Luk 24:37[onaninso: opa]

OPSINJIKA (oppressed)amasiye ndi opsinjika...Mas 10:18mwa chilungamo onse opsinjika...Mas 103:6kwa anthu owapsinja .Mas 72:14

OPUSA (foolish)paja anthu anga ndi opusa...Yer 4:22Agalatiya opusa inu...Agal 3:1kale ifenso tinali opusa...Tit 3:3ndife opusa chifukwa cha Khristu...1 Akor 4:10[onaninso: wopusa, zopusa]

OPUSA (foolishness)maganizo opusa ndiwo tchimo...Miy 24:9mtanda ndi chinthu chopusa...1 Akor 1:18[onaninso: chibwana, kupusa, zopusa]

OSABALA OFULIDWA (eunuchs)osabala amene anazifula okha...Mat 19:12

OSACHIMWA (innocent)anthu osachimwa adzagawana...Yob 27:17[onaninso: wosalakwa]

OSAKHULUPIRIKA (unfaithful)munthu wosakhulupirika...Miy 13:15[onaninso: oipa]

OSAKHULUPIRIRA (unbelievers)kwa anthu osakhulupirira...1 Akor 14:22osadziwa kapena osakhulupirira...1 Akor 14:23

OSALUNGAMA (unjust)osalungama akuchitabe zoipa...Zef 3:5osalungama ndi adama...Luk 18:11olungama ndi osalungama...Mac 24:15m’malo mwa osalungama...1 Pet 3:18[onaninso: oipa, wonyenga, wosalungama]

Page 127: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

OSALUNGAMA (unrighteous)osalungama asinthe...Yes 55:7m’chuma cha osalungama...Luk 16:11anthu osalungama sadzaulawa...1 Akor 6:9

OSAMVERA (disobedient)mtundu wa anthu osandimvera...Aro 10:21tinali opusa, osamvera...Tit 3:3ndi mau, pokhala osamvera...1 Pet 2:8imene inakhala yosamvera kale...1 Pet 3:20

OSAPHUNZIRA (uneducated)anthu wamba, osaphunzira...Mac 4:13

OSAUKA (afflicted)kufuula kwa osauka...Yob 34:28masiku onse a osauka...Miy 15:15[onaninso: sautsa,sautsidwa, zunzika]

OSAUKA (poor)ena osauka, osowa zinthu...Deut 15:11chisoni anthu osauka...Yob 30:25mudapatsa anthu osauka...Mas 68:10osauka ndi osowa...Mas 74:21anthu osauka awatulutsa...Mas 107:41amagulitsa anthu osauka...Amo 2:6anthu osauka muli nao...Mat 26:11[onaninso: mphawi, wosauka]

OSWEKAMTIMA (broken hearted)achiritsa osweka mtima...Mas 147:3

OTSUTSANA (adversaries)udzaononga otsutsana...Aheb 10:27[onaninso: adani, vuta]

OWERENGEKA (few)amakhala masiku owerengeka...Yob 14:1masiku ake akhale owerengeka...Mas 109:8mau ako akhale owerengeka...Mlal 5:2amene amaipeza ndi owerengeka...Mat 7:14adzapulumuka ndi anthu owerengeka...Luk 13:23m’chombomo anthu owerengeka...1 Pet 3:20[onaninso: chepa]

OZUNZIKA (humble)saiwala kulira kwa ozunzika...Mas 9:12musaiwale ozunzika...Mas 10:12mwamva chikhumbo cha ozunzika...Mas 10:17anthu ozunzika ndi osauka...Zef 3:12[onaninso: chepetsa, odzichepetsa, ofatsa, wodzichepetsa,wofatsa]

P

PACHIKA (crucified)anampachika pamtanda...Luk 23:33mwampachika ndi kumupha...Mac 2:23akadadziwa sakadampachika Mbuye...1 Akor 2:8[onaninso: pachikidwa]

PACHIKA (crucify)mpachikeni pamtanda...Marko 15:13ulamuliro wakukupachikani...Yoh 19:10adzipachikanso okha...Aheb 6:6

PACHIKIDWA (crucified)apachikidwe pamtanda...Mat 27:22unapachikidwa limodzi ndi iye...Aro 6:6kodi Paulo anapachikidwa chifukwa...1 Akor 1:13

Yesu Khristu, ndi iye wopachikidwa...1 Akor 2 :2pakuti adapachikidwa muufooko...2 Akor 13:4ndinapachikidwa ndi Khristu...Agal 2:20[onaninso: pachika]

PACHIKIDWA (hang)wopachikidwa pa mtengo...Deu 21:23nadzipachika yekha...Mat 27:5

PACHIKIDWA (hanged)aliyense wapachikidwa...Agal 3:13

PADANI ARAMU (Padan Aram)chimodzimodzi ndi Mesopotamia...Gen 24:10kwao kwa mkazi wa Isaki...Gen 25:20Yakobo anathawirako...Gen 28:2-7Yakobo anabwerera kuchokera...Gen 31:17,18anthu ake otchedwa Asiriya...Gen 31:24chilankhulo chao chotchedwa Chiaramu...2 Maf 18:26

PAFOSI (Paphos)Paulo anampangitsa khungu Elemasi kumeneko...Mac 13:6-13

PAFUPI (almost)koma ine ndinali pafupi...Mas 73:2iyeyi adaali pafupifupi kufa...Afil 2:30a Mosewo pafupifupi...Aheb 9:22

PAFUPI (hand)kodi ndine Mulungu wapafupi...Yer 23:23[onaninso: dzanja, manja, mkono, yandikira]

PAFUPI (near)wakukhala ndi Mulungu pafupi...Deut 4:7mauwa ali pafupifupi ndi inu...Deut 30:14Yehova ali pafupi ndi...Mas 145:18pamene ali pafupi...Yes 55:6kuti iye ali pafupi...Mat 24:33ufumu wa Mulungu uli pafupi...Luk 21:31mau ali pafupi ndi iwe...Aro 10:8mtendere kwa iwo a pafupi...Aef 2:17zichitike zonsezi ili pafupi...Chiv 1:3

PAKA (anoint)ndi mankhwala opaka m’maso mwako kuti ukaone...Chiv 3:18[onaninso: dzola, dzoza]

PAKAMWA (mouth)adapatsa munthu pakamwa...Eks 4:11m’kamwa mwa makanda...Mas 8:2pakamwa pake pamatuluka...Mas 37:30pakamwa panga padzanena...Mas 49:3chonse chitseka pakamwa...Mas 107:42mkamwa mwa chitsiru...Miy 10:14wogwira pakamwa pake...Miy 13:3mkamwa mwa mkazi...Miy 22:14pakamwa poshashalika...Miy 26:28munthu ndiponso pakamwa...Dan 7:5aliyense achenjere ndi pakamwa...Mik 7:5cholowa m’kamwa mwa munthu...Mat 15:11pakamwa pako ndikuweruza...Luk 19:22inu kamwa ndi nzeru...Luk 21:15uvomereza ndi pakamwa pako...Aro 10:9chakecho ndi pakamwa...Aro 10:10ndidzakulavula m’kamwa...Chiv 3:16

PAKATI (midst)Mulungu ali mkati mwake...Mas 46:1kuti ine ndili pakati...Yow 2:27ndili komweko pakati...Mat 18:20

PALIDWA UBWENZI (betrothed)

Page 128: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

mudzapalana ubwenzi ndi mkazi...Deut 28:30kwa namwali wopalidwa ubwenzi...Luk 1:27ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna...2 Akor 11:2

PALITI (Palti, Paltiel)mwamuna yemwe Saulo anampatsa Mikala, mkazi wa Davide,1 Sam 25:44; 2 Sam 3:15

PAMASO (presence)ndi mkazi wake pamaso pa Yehova...Gen 3:8Kaini adachoka pamaso pa...Gen 4:16tiferenji pamaso panu...Gen 47:15pamaso pa munthu wa imvi...Lev 19:32mantha kwambiri pamaso pa...Yob 23:15adzakhala pamaso pake...Mas 140:13simunjenjemera pamaso panga...Yer 5:22zidzanjenjemera pamaso panga...Ezek 38:20chete, pamaso pa Ambuye...Zef 1:7tinadya ndi kumwa pamaso panu...Luk 13:26ndi kukondwera pamaso panu...Mac 2:28[onaninso: nkhope]

PAMBANA (overcome)chifukwa mwapambana...1 Yoh 2:13okhulupirika nawonso adzapambana...Chiv 17:14[onaninso: gonjetsa, laka]

PAMBANA (better)zipambana ndi katundu wambiri...Miy 15:16[onaninso: posa]

PAMBANA (excels)kuti nzeru ipambana utsiru...Mlal 2:13munthu sapambana...Mlal 3:19cha ulemelero wopambanawu...2 Akor 3:10[onaninso: chita mwaluso]

PAMBUYO PAKE (afterward)pambuyo pake adzakulolani...Eks 11:1pambuyo pake mudzandilandira...Mas 73:24ndipo pambuyo pake...1 Akor 15:23

PAMFILIYA (Pamphylia)anthu ochokerako analipo patsiku la Pentekosite...Mac 2:10Paulo anapitako, ndi kumene Yohane Marko anabwerera kupitakwao...Mac 13:13;15:38Paulo analalikira m’mizinda yake...Mac 14:24,25

PAMWAMBA (above)pamwamba pa iye...Yes 6:2amene ali pamwamba pa onse...Aef 4:6[onaninso: kumwamba, m’mwamba, posa]

PAMWAMBA (pinnacle)anamuika Iye pamwamba...Luk 4:9

PANDA PAKE (futile)sichikhala kwa inu chinthu chopanda pake...Deut 32:47Miyambo ya anthu amitundu inayo njopanda pake...Yer 10:3za anzeru, kuti ziri zopanda pake...1 Akor 3:20chikhulupiriro chanu chili chopanda pake...1 Akor 15:17

PANDA PAKE (futility)andilowetsa miyezi yopanda pake...Yob 7:3[onaninso: chabe, utsiru]

PANDA CHILEMA (blameless)oyera ndi opanda chilema...Akol 1:22zopanda chilema...1 Ates 5:23woyang’anira akhale wopanda chilema...1 Tim 3:2akakhala opanda chilema...1 Tim 3:10opanda banga ndi opanda chilema...2 Pet 3:14

[onaninso: khala wosalakwa, ngwiro, opanda chilema]

PANDA (beat)ndidzapandanso odana naye...Mas 89:23[onaninso: guguda, menya, puntha]

PANDA (strike)akandipanda munthu wolungama...Mas 141:5nadzapanda mafunde a m’nyanja...Zek 10:11koma ngati bwino undipandiranji...Yoh 18:23ndi kupanda dziko ndi mliri ulionse...Chiv 11:6[onaninso: kantha, menya, tentha, wamba]

PANDA (struck)napanda thanthwe kawiri...Num 20:11pakuti mwapanda adani anga...Mas 3:7taonani anapanda thanthwe...Mas 78:20nampanda Iye pamutu...Mat 27:30talota anakupanda Iwe ndani...Luk 22:64[onaninso: kantha, menya]

PANDUKA (rebel)koma mukana ndi kumapanduka...Yes 1:20[onaninso: galukira, pikisana, ukira]

PANDUKIRA (rebellion)akulalikira zopandukira...Yer 28:16[onaninso: galukira, ukira]

PANDUKIRA (rebellious)anthu ondipandukirawa...Yes 65:2ndiponso a mtima waupandu...Yer 5:23[onaninso: ukira]

PANGA (made)ndani wapanga mulungu...Yes 44:10za iye amene anachipanga...Yes 29:16chinthu chopangidwa chidzanena...Aro 9:20ndi amene anachipanga...Aro 9:20onaninso: chita, lenga]

PANGA (make)tipange munthu nchifanizo chathu...Gen 1:26Mulungu ndipo adapangira...Gen 3:21ndipo tidzipangire ife tokha...Gen 11:4usadzipangire iwe wekha fano...Eks 20:4[onaninso: chita, lenga]

PANGANA (agreed)adzayenda pamodzi asanapanganiranetu...Amo 3:3napangana naye kumpatsa ndalama...Luk 22:5[onaninso: vomereza]

PANGANA (covenanted)monga ndinapangana...2 Mbir 7:18monga momwe ndinapangana nanu...Hagai 2:5pamodzi asanapanganiranetu...Amo 3:3napangana naye kumpatsa...Luk 22:5

PANGANO (convenant)ndidzakhazikitsa ndi iwe pangano...Gen 6:18pangano langa liri ndi iwe...Gen 17:4likhale pangano losatha...Eks 31:16ndilo pangano lamchele wosatha...Num 18:19adzawadziwitsa pangano lake...Mas 25:14ukhale pangano la anthu...Yes 42:6imvani mau a pangano...Yer 11:2ndidzapangana pangano latsopano...Yer 31:31ndinapangana mapangano...Yer 34:13kuti ndiphwanye pangano...Zek 11:10chikho ichi ndi pangano latsopano...Luk 22:20silifafaniza pangano...Agal 3:17

Page 129: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ali Nkhoswe ya pangano...Aheb 8:6[onaninso: chipangano]

PANSI (beneath)ndi padziko lapansi palibe wina...Deut 4:39inu ndinu wochokera pansi...Yoh 8:23

PANSI (world)chifukwa ana a nthawi ya pansi pano ali a nzeru...Luk 16:8musafanizidwe ndi makhalidwe a pansi pano...Aro 12:2[onaninso: dziko, dziko lapansi]

PARADAISO (Paradise)udzakhala ndine m’Paradaiso...Luk 23:43Kunka ku Paradaiso...2 Akor 12:4moyo umene uli m’Paradaiso...Chiv 2:7

PARAMULA (offend)adzayesedwa oparamula...Yer 2:3[onaninso: khumudwitsa, lakwa]

PARANI (Paran)malo a Aismaele amene anali ku ukapolo...Gen 21:21Aisraeli anamanga zithando zao kumeneko...Num 10:12Kulikulu kwa zothira mu ndiwo zokometsera...Num 13:3,26kumene Davide anathawirako...1 Sam 25:1

PARMENASI (Parmenas)m’modzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:5

PASANAFIKE (beforehand)ndakuuziranitu zinthu zonse zisanafike...Marko 13:23usanafike mlandu...Luk 21:14

PASKA (Passover)limeneli ndilo tsiku la Paska...Eks 12:11Paska imeneyi adzaichitira kuti...2 Maf 23:23kwanu kuno pwando la Paska...Mat 26:18mwanawankhosa wathu wa Paska...2 Akor 5:7chikondwerero cha Paska...Aheb 11:28

PASULA (destroy)kudzapasula chilamulo...Mat 5:17usapasule ntchito ya Mulungu...Aro 14:20ya msasa wathu ipasuka...2 Akor 5:1[onaninso: ononga]

PASULA (destruction)kupulumutsa pena kupasula m’malire ako...Yes 60:18[onaninso: chiwonongeko, khala fumbi, ononga, onongeka]

PASURI (Pashhur)Mdindo amene anatsutsa Yeremiya...Yer 21:1;38:1-3— wansembe yemwe anaika Yeremiya mndende...Yer 20:1-6

PATALI (far)inu muli chapatali ndithu...Eks 24:1ndikakhala patali...Yer 23:23Abrahamu ali patali...Luk 16:23adangoziwonera chapatali...Aheb 11:13[onaninso: kutali]

PATHUPI (conceived)mai wanga adatenga pathupi...Mas 51:5[onaninso: badwa, ima]

PATIMOSI (Patmos)Yohane anaponyedwako kuti asathenso kubwerera ku tsidyalina...Chiv 1:9

PATIROSI (Pathros)unakambidwa kukhala ufumu waung’ono...Ezek 29:14-16kothawirako kwa Ayuda omwe anabalalika...Yer 44:1-15

Ayuda anayenera kusonkhanitsidwa pamodzikuchokera kumeneku...Yes 11:11

PATSA MONI (greet)ngati mupatsa moni abale okha...Mat 5:47mupatse moni mwachikondi...1 Akor 16:20musampatse ndi moni yemwe...2 Yoh 10[onaninso: pereka moni]

PATSA (bestowed)chikondicho Atate watipatsa...1 Yoh 3:1

PATSA (gave)ameneyo anandipatsa...Gen 3:12ndani anakupatsani ulamuliro...Mat 21:23kuti anapatsa mwana...Yoh 3:16amene mwandipatsa...Yoh 17:12onaninso: pereka]

PATSA (give)mundipatse tsono nzeru ndi chidziwitso...2 Mbir 1:10muwapatse monga mwa ntchito zao...Mas 28:4Iye adzakupatsani zokhumba za mtima wanu...Mas 37:4Yehova adzapereka zokoma...Mas 85:12undipatse mtima wako...Miy 23:26mudzapatsa kwa Yakobo choonadi...Mik 7:20iye wopempha iwe umpatse...Mat 5:42mutipatse ife lero...Mat 6:11kagulitse zomwe uli nazo, nupatse...Mat 19:21ine ndidzapatsa inu ulamuliro...Luk 4:6Ine ndidzapatsa moyo wosatha...Yoh 10:28ndikupatsani inu lamulo latsopano...Yoh 13:34chimene ndili nacho, ichi ndikupatsa...Mac 3:6[onaninso: pereka]

PATSA (given)munthu aliyense adampatsa...Luk 12:48ichi chonse iye anandipatsa ine...Yoh 6:39[onaninso: patsidwa]

PATSA (gives)amene amapatsa osauka sadzasowa...Miy 28:27wabwino ampatsa nzeru ndi chidziwitso...Mlal 2:26kuchokera kumwamba ndi kupatsa moyo...Yoh 6:33chimene anandipatsa Atate...Yoh 6:37mtendere wanga ndikupatsani...Yoh 14:27Mulungu amene atipatsa zonse...1 Tim 6:17Mulungu amene apatsa kwa onse...Yak 1:15Mulungu apatsa chisomo choposa...Yak 4:6koma apatsa chisomo odzichepetsa...Yak 4:6[onaninso: taya]

PATSA (grant)tipatseni chipulumutso...Mas 85:7ndidzampatsa akhale pansi...Chiv 3:21[onaninso: lamulira]

PATSA (provide)Mulungu akatipatsa mwana wankhosa...Gen 22:8angathenso kutipatsa ife anthu ake...Mas 78:20ndaupatsa madalitso ndi zokoma...Yer 33:9wina aliyense sawapatsa...1 Tim 5:8

PATSA (provides)khwangwala amampatsa chakudya...Yob 38:41

PATSA (supplies)amene amapatsa mbeu...2 Akor 9:10anakupatsani Mzimu Woyera...Agal 3:5Yesu adzakupatsani zonse...Afil 4:19

PATSANSO MOYO (revive)

Page 130: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kodi simudzatipatsanso moyo...Mas 85:6mundipatse moyo monga mwa...Mas 119:25[onaninso: tsitsimutsa]

PATSIDWA (given)amene ali nazo, kudzapatsidwa kwa iye...Mat 13:12kudzapatsidwa ndipo iye adzakhala nazo...Mat 25:29tikadziwe zimene zipatsidwa kwa ife...1 Akor 2:12[onaninso: patsa]

PATUKA (depart)nupatuke pa zoipa...Miy 3:7[onaninso: choka, futuka]

PATUKANA (parted)kotero anapatukana...Mac 15:39[onaninso: lekana]

PATULA (exclude)nadzapatula inu...Luk 6:22

PATULANA (divisions)pasakhale kupatulana...1 Akor 1:10mumapatulana...1 Akor 11:18[onaninso: mipatuko]

PATULIKA KOPAMBANA (holiest)m’malo opatulika kopambana...Aheb 9:8m’malo opatulika kopambana...Aheb 10:19

PATULIKA (holiness)ndipo idzatchedwa njira yopatulika...Yes 35:8[onaninso: chiyeretso, chiyero, woyera]

PATULIKA (holy)wopatulika wadzisokoneza ndi...Ezara 9:2yense ndi opatulika...Aro 11:16ndi kumpsopsona kopatulika...Aro 16:16m’malo opatulika...Aheb 9:24[onaninso: woyera, yera]

PATULIRA (set apart)kuti uzikapatulira...Eks 13:12wadzipatulira iye yemwe anthu...Mas 4:3

PATURA (consecrate)ndipatulire ine yense woyamba kubadwa...Eks 13:2kudzipatulira kwa Yehova lero...1 Mbir 29:5patulani tsiku losala...Yow 2:15[onaninso: pereka]

PATURA (consecrated)ndapatula nyumba imene waimangayi...1 Maf 9:3

PAULO SERGIO (Sergius Paulus)bwanamkubwa wachiroma wa ku Kipro...Mac 13:4,7

PAULO (Paul)mzika ya ku Roma yochokera ku Tasasi; anaphunzitsidwa ndiGamalieli...Mac 22:3,25-28dzina lake loyamba linali Saulo; anazunza mpingo...Mac7:58;8:1,3;9:1,2anatembenuka mtima panjira yopita ku Damasiko...Mac 9:3-19analalikira ku Damasiko; anathawira ku Yerusalemu kenako kuTasiko...Mac 9:20-30anatumikira ku Antiokeya; anatumizidwa ku Yerusalemu...Mac11:25-30ulendo wake wokatumikira woyamba...Mac 13;14alankhulira Amitundu ku bwalo la ku Yerusalemu...Mac 15:1-5,12ulendo wake wachiwiri wokatumikira...Mac 15:36— 18:22ulendo wake wokatumikira wachitatu...Mac 18:23-21:14anamangidwa ku Yerusalemu,

kudziteteza kwake pamaso pa akuluakulu achiroma...Mac 21:15-26:32anatumizidwa ku Roma...Mac 27:1-28:31Makalata ake; Aroma, 1 ndi 2 Akorinto, Agalatiya, Aefeso,Afilipi, Akolose,1 ndi 2 Atesalonika, 1 ndi 2 Timoteo, Tito, Filemoni.

PEKA (Pekah)mwana wa Remaliya, analanda ufumu wa Israelimwaupandu...2 Maf 15:25-28anapanga mgwirizano ndi Rezini wa ku Siriya kutsutsana ndiAhazi...Yes 7:1-9mgwirizano wao unagonjetsedwa; akapolo anabwerera kwao...2Maf 16:5-9dera lake linalamulidwa ndi Tigilati-Pelesele...2 Maf 15:29anaphedwa ndi Hoseya...2 Maf 15:30

PEKAHIYA (Pekahiah)mwana wa Menahemu; mfumu ya Israeli...2 Maf 15:22-26anaphedwa ndi Peka..2 Maf 15:23-25

PEMBEDZA (beg)ndikadangompembedza wondiweruza ine...Yob 9:15[onaninso: dandaulira, pempha]

PEMBEDZA (entreated)wa Mulungu anapembedza Yehova...1 Maf 13:6[onaninso: pempha]

PEMBEDZA (worship)bwerani timpembedze...Mas 95:6motero tabwera kudzampembedza...Mat 2:2mukagwada pansi ndi kundipembedza...Mat 4:9amandipembedza inde...Mat 15:9Asamariyanu mumapembedza...Yoh 4:22adzapembedza Atate mwauzimu...Yoh 4:23mumapembedza wosamdziwayo...Mac 17:23ndimapembedza Mulungu wa...Mac 24:14popembedza amatamanda angelo...Akol 2:18onse a Mulungu azimpembedza...Aheb 1:6ndi kupembedza wokhala ndi...Chiv 4:10[onaninso: gwadira, lambira, pemphera]

PEMBEDZA (worshiped)anthu akapembedza Mulungu...Yoh 4:20adadzigwetsa pansi mowerama, napembedza...Chiv 5:14adadzigwetsa chafufumimba napembedza...Chiv 11:16napembedza Mulungu...Chiv 19:4

PEMBEDZERA (entreat)undipembedzere Yehova Mulungu wako...1 Maf 13:6

PEMBEDZERA (intercede)Yehova, adzampembedzera ndani...1 Sam 2:25ambiri, napembedza olakwa...Yes 53:12Mzimu mwini atipembedzera...Aro 8:26chikhalire wakuwapembedzera...Aheb 7:25

PEMBEDZO (prayer)akumva pembedzo lao...1 Pet 3:12[onaninso: mapemphero]

PEMPHA (appeal)ndikupempha kuti mlandu wangawu...Mac 25:11makamaka ndingochita kupempha...Fil 9

PEMPHA (beg)ndikadangompembedza wondiweruza ine...Yob 9:15kupemphapempha kundichititsa manyazi...Luk 16:3[onaninso: dandaulira, pembedza]

PEMPHA (beseech)bwererani tikupemphani...Mas 80:14

Page 131: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

chifukwa chake ndikupemphani inu...Aro 12:1chifukwa chotumidwa ndi Ambuye, ndikupemphani...Aef 4:1

PEMPHA (entreat)tayesani kupempha Mulungu...Mal 1:9ponamizidwa tipempha...1 Akor 4:13[onaninso: umiriza]

PEMPHA (entreated)tinasala ndi kupempha ichi...Ezara 8:23[onaninso: pembedza]

PEMPHA (plead)pita msanga ukapemphe...Miy 6:3[onaninso: nenera, pemphero, tsutsana, weruza]

PEMPHA (pray)ndipo Ine ndidzapempha Atate...Yoh 14:16[onaninso: dandaula, pemphera, pempherera]

PEMPHERA (pray)pamene mukupemphera...Mat 6:5pamene ukuti upemphere...Mat 6:6pempherani inu chomwechi...Mat 6:9popemphera muziti...Mat 26:41adakwera kuphiri kukapemphera...Marko 6:46Yesu ankapemphera...Luk 11:1azipemphera nthawi zonse...Luk 18:1ndidzapemphera ndi mtima wanga...1 Akor 14:15muzipemphera kosalekeza...1 Ates 5:17popemphera azikweza manja ao...1 Tim 2:8akumva zowawa? Apemphere...Yak 5:13ali m’mavuto, apemphere...Yak 5:16losadzetsa imfa, apemphere...1 Yoh 5:16ndimapemphera kuti zako zonse...3 Yoh 2[onaninso: dandaula, pempha, pempherera]

PEMPHERA (prayed)adaimirira nayamba kupemphera...Luk 18:11nkumapemphera kolimba koposa...Luk 22:44iye uja adaapemphera kolimba...Yak 5:17

PEMPHERA (prayer)ndikupemphera Mulungu...Mas 42:8mutayamba mwapemphera...Mat 17:21ku phiri kukapemphera...Luk 6:12ntchito ya kupemphera...Mac 6:4muzipemphera nthawi zonse...Aro 12:12chitani zonse mopemphera...Aef 6:18[onaninso: pempherera, pemphero]

PEMPHERA (worship)ndipo tikapemphera ndi kubwerako...Gen 22:5[onaninso: gwadira, lambira, pembedza]

PEMPHERERA (pray)pakuleka kukupemphererani...1 Sam 12:23ndipo mudziwapempherera...Mat 5:44Ine ndiwapempherera iwo...Yoh 17:9sindikupempherera anthu ena...Yoh 17:20m’mene tiyenera kupempherera...Aro 8:26abale muzipempherera...1 Ates 5:25[onaninso: dandaula, pempha, pemphera]

PEMPHERERA (prayer)pamene ndikuwapempherera...Mas 109:4kuli malo opemphererako...Mac 16:13ankapempherera ndi chikhulupiriro...Yak 5:15[onaninso: pemphera, pemphero]

PEMPHERO (plead)ndi pemphero langa ndi loyera...Yob 16:21

[onaninso: nenera, pemphera, tsutsana, weruza]

PEMPHERO (prayer)mumve kumwambako pemphero...1 Maf 8:45ndidzatchera khutu ku pemphero...2 Mbir 7:15pemphero langa kwa Mulungu...Yob 16:17ndipo pemphero langa linabwera...Mas 35:13pemphero langa lifike...Mas 88:2koma pemphero la anthu...Miy 15:8muzipereke ku mapemphero...1 Akor 7:5koma m’mapemphero anu...Afil 4:6Mulungu ndi mapemphero...1 Tim 4:5[onaninso: pemphera, pempherera]

PENTEKOSTE (Pentecost)la Pentekoste lidafika...Mac 2:1

PENI (pen)lilime langa ndilo peni yofulumiza kulemba...Mas 45:1peni lonyenga la alembi lichita zonyenga...Yer 8:8tchimo la Yuda lalembedwa ndi peni lachitsulo...Yer 17:1komatu sindifuna kulembera ndi kapezi ndi peni...3 Yoh 1:13[onaninso: chozokotera]

PENUWELE (Penuel)malo ena kummwera kwa Yordane; malo omwe Yakoboanalimbana ndi mngelo,Gen 32:24-31anthu okhalamo anaphedwa ndi Gidiyoni...Ower 8:8,9

PENYA (look)ndipo adzandipenyera ine...Zek 12:10popeza sitipenyerera zinthu...2 Akor 4:18koma yense apenyererenso...Afil 2:4mudzipenyerere nokha...2 Yoh 8[onaninso: cheuka, penya, yang’ana]

PENYA (looked)anapenya pansi ali kumwamba...Mas 102:19[onaninso: penyerera, yang’ana]

PENYERERA (attention)ndipo mukapenyerera iye wovala...Yak 2:3[onaninso: mvetsa, samalira]

PENYERERA (looked)pakuti anapenyerera...Aheb 11:26[onaninso: penya, yang’ana]

PENYETSETSA (observe)upenye munthu wopanda...Mas 37:37maso ako apenyetsetse...Miy 23:26[onaninso: ona, sunga]

PEORI (Peor)phiri la Moabu loyang’anana ndi Yeriko...Num 23:28zithando za Israeli zimaoneka kuchokera...Num 24:2— mulungu wa a Moabu wotchedwa Baala wa Peori...Num25:3,5,18Aisraeli analangidwa chifukwa chompembedza...Num 31:16

PEPULA (reject)mupepula onse akusokera m’malemba...Mas 119:118[onaninso: kaniza, nyoza]

PEPUTSA (despise)kodi kapena ukupeputsa chifundo...Aro 2:4[onaninso: nyazitsa, nyoza]

PEPUTSA (despises)wopeputsa mnzake asowa nzeru...Miy 11:12[onaninso: nyoza]

Page 132: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

PEPUTSA (dishonour)ndipo inu mundipeputsa...Yoh 8:49[onaninso: manyazi, mnyozo, zopanda ulemu]

PEPUTSA (dishonours)mwana wamwamuna apeputsa...Mika 7:6[onaninso: nyoza]

PEPUTSA (humiliation)adampeputsa, pa mlandu wake sadamchitire chilungamo...Mac8:33[onaninso: tsitsa, chititsa manyazi]

PEREKA KWA ADANI (betraying)si uyu wodzandipereka uja...Mat 26:46mongadi ukupereka mwana wa munthu...Luk 22:48adzakuperekani kwa adani anu ndani...Yoh 21:20

PEREKA KWA ADANI (betray)musatipereke ife anthu othawa nkhondo...Yes 16:3wina mwa inu andipere...Mat 26:21mbale adzidzapereka mbale wake...Marko 13:12

PEREKA MONI (greet)upereke moni kwa abwenzi onse...3 Yoh 14[onaninso: patsa moni]

PEREKA (commit)pereka zochita zako kwa Yehova...Miy 16:3m’manja mwanu ndipereka...Luk 23:46[onaninso: chita]

PEREKA (consecrate)uzipereka chiperekere phindu lao...Mika 4:13[onaninso: patura]

PEREKA (gave)amene anadzipereka yekha...Agal 1:4nadzipereka yekha chifukwa...Agal 2:20nadzipereka yekha m’malo mwake...Aef 5:25nyanja inapereka akufawo...Chiv 20:13onaninso: patsa]

PEREKA (give)koma anampereka chifukwa cha...Aro 8:32Mulungu akonda wopereka mokondwa..2 Akor 9:7[onaninso: patsa]

PEREKA (offer)pamene mupereka, mupereka yakhungu...Malak 1:8pamenepo idza nupereke mtulo wako...Mat 5:24tipereke chiperekere nsembe...Aheb 13:15

PEREKA (offered)anadzipereka yekha...Aheb 9:14m’mene adapereka nsembe...Aheb 10:12Abele anapereka kwa Mulungu...Aheb 11:4[onaninso: perekedwa]

PEREKEDWA (betrayed)mwana wa munthu akudzaperekedwa...Mat 17:22usiku umene adaperekedwa uja...1 Akor 11:23

PEREKEDWA (dedicated)zilizonse zoperekedwa chiperekere...Ezek 44:29

PEREKEDWA (delivered)amene anaperekedwa chifukwa...Aro 4:25adzapereka ufumu kwa Mulungu...1 Akor 15:24[onaninso: landitsa, pulumutsa]

PEREKEDWA (devoted)chinthu chilichonse choperekedwa...Lev 27:28zilizonse zoperekedwa chiperekere...Num 18:14ndiye wodzipereka...Mas 119:38

PEREKEDWA (offered)kudya zoperekedwa nsembe...1Akor 8:10Khristunso anaperekedwanso...Aheb 9:28[onaninso: pereka]

PEREZI (Perez)mmodzi wa ana a mapasa a Yuda kudzera mwa Tamara...Gen38:24-30

PERGAMO (Pergamus)dera la umodzi mwa mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 1:11uthenga wake wapaderadera...Chiv 2:12-17

PETRO (Peter)msodzi wa nsomba, anaitanidwa kutsata Yesu...Mat4::18-20;Yoh 1:40-42.anaitanidwa kukhala mtumwi...Mat 10:2-4anayenda pamadzi...Mat 14:28-33anavomereza za chimene Yesu anali...Mat 26:69-75analamulidwa ndipo anatumidwa kuti adyetse nkhosa zaKhristu...Yoh 21:15-17anatsogolera ophunzira a Yesu...Mac 1:15-26analalikira pa tsiku la Pentekoste...Mac 2:1-41anapanga zodabwitsa...Mac 3:1-11;5:14-16;9:32-43anaitanidwa kukatumikira kwa amitundu...Mac 10anadziteteza kuyendera amitundu kwake...Mac 11:1-18anamangidwa ndi kuomboledwa...Mac 12:3-19analankhula pamsonkhano wa ku Yerusalemu...Mac 15:7-14analemba kalata zake...1 Pet 1:1;2 Pet 1:1

PEWA (abstain)mupewe maonekedwe...1 Ates 5:22[onaninso: kaniza, letsa, lewa]

PEZA (find)tchimo lanu lidzakupezani...Num 32:23kwa omwe awapeza...Miy 4:22udzazipeza popita masiku...Mlal 11:1funani ndipo mudzapeza...Mat 7:7chifukwa cha Ine, udzaupeza...Mat 10:39adzampeza iye ali kuchita...Mat 24:46mudzapeza mwana wakhanda...Luk 2:12ndilibe kupeza chifukwa...Luk 23:4chotero ndipeza lamulo ili...Aro 7:21chifundo ndi kupeza chisomo...Aheb 4:16ndipo posaupeza...Luk 11:24

PEZA (finds)wondipeza ine apeza moyo...Miy 8:35wopeza mkazi apeza...Miy 18:22dzanja lako lichipeza…Mlal 9:10ndi wakufunayo apeza...Mat 7:8Iye amene apeza moyo wake...Mat 10:39ndi wakufunayo apeza...Luk 11:10

PEZA (found)kwa Adamu sadapezedwa...Gen 2:20nzeru idzapezeka kuti...Yob 28:12pa nthawi yakupeza inu...Mas 32:6ndapeza Davide mtumiki wanga...Mas 89:20m’modzi wa chikwi ndinampeza...Mla 7:28ichi chokha ndachipeza...Mla 7:29ndinampeza amene moyo wanga...Nyi 3:4Yehova popezeka Iye...Yes 55:6zipatso zako zipezeka...Hos 14:8koma anapeza palibe…Luk 13:6anali wotayika ndipo wapezeka...Luk 15:24

Page 133: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

tapeza ife Mesiya...Yoh 1:41ndinalipeza lakupatsa imfa...Aro 7:10ndikupezedwa mwa iye...Afil 3:9mupezedwe ndi iye mumtendere...2 Pet 3:14

PEZA (obtain)ndipo simukhoza kupeza...Yak 4:2[onaninso: khala, lamdira]

PHALE (potsherd)Yobu adatenga phale...Yob 2:8kwauma ngati phale...Mas 22:15ngakhale ali ngati phale...Yes 45:9

PHAPHATIZA (narrow)pa chipata chophaphatiza...Mat 7:13chobwera kumoyo nchophaphatiza...Mat 7:14

PHAZI (feet)aiwalika ndi phazi...Yob 28:4osalola phazi lathu literereke...Mas 66:9nsapato yako ku phazi...Yes 20:2afike pa phazi lake...Yes 41:2kapena phazi lako likakukhumudwitsa...Mat 18:8[onaninso: mapazi, miyendo]

PHAZI (foot)phazi lako kuti literereke...Mas 121:3phazi lako silidzaphunthwa...Miy 3:23kuchokera ku phazi mpaka...Yes 1:6ukaletsa phazi lako...Yes 58:13kapena phazi koposa...Mat 18:8ungagunde konse phazi...Luk 4:11phazi likati, popeza...1 Akor 12:15

PHESI (straw)ngati phesi louluka...Yob 21:18[onaninso: ziputu]

PHIKA (bake)ndi wophika mkate wake...Gen 40:1ndikuphika timitanda khumi...Lev 24:5

PHIKA (cooked)manja a akazi achisoni anaphika...Malio 4:10

PHIKO (wing)phiko limodzi la Kerubi...1 Maf 6:24[onaninso: chofunda]

PHIMBA (cover)ndikukuphimba ndi dzanja langa...Eks 33:22[onaninso: kuta, vundikira]

PHIMBA (covered)awiri anaphimba napo nkhope...Yes 6:2mtambo uwaphimbe...Mas 105:39kwa iye ngati chophimba...1 Akor 11:15[onaninso: kuta, phimba]

PHINDU (interest)usamuwerengere phindu...Eks 22:25sanandikongoletsa pa phindu...Yer 15:10anthu opanda nawo phindu...Yes 30:5ndikanaitenga ndi phindu...Luk 19:23pali phindu lanjinso pakuumbala...Aro 3:1Khristu simupindula nayenso...Agal 5:2kutero kulibe phindu...2 Tim 2:14amatilanga kuti tipindule...Aheb 12:10

PHINDU (profit)zinali zopanda phindu...Mlal 2:11phindu lake lopeza...Ezek 22:13

pali phindu lanji kumatsata...Mal 3:14pali phindu lanjinso pakuumbala...Aro 3:1kutero kulibe phindu...2 Tim 2:14pali phindu lanji ngati munthu...Yak 2:14[onaninso: pindula]

PHINDU (profitable)munthu nkukhala waphindu...Yob 22:2kunyada kwake nkopanda phindu...2 Akor 12:1ankanena kuti palibe phindu...Yob 34:9[onaninso: pindulitsa]

PHINDU (prosper)akukonda inu adzaona phindu...Mas 122:6[onaninso: dalitsa, lemera, lemereza]

PHIRI LA ZIYONI (Mount Zion)otsalawo adzatuluka kuchokera pamenepa...2 Maf 19:31

PHIRI LA TABORI (Mount Tabor)Debora anatumiza Baraki kumeneku kukagonjetsaAkanani...Ower 4:6-4

PHIRI LA GILEADI (Mount Gilead)Gideoni anagawa anthu a nkhondo pamenepa...Ower 7:3

PHIRI LA KARIMERE (Mount Carmel)aneneri anasonkhanapo...1 Maf 18:19,20Elisa anapitako...2 Maf 2:25Mzimayi wa Sunami anapita kwa Elisa pamalo amenewa...2Maf 4:25

PHIRI LA GERAZIMU (Mount Gerizim)phiri la madalitso...Deut 11:29;27:12Yotamu adalankhula ndi anthu a ku Sekemu pamenepa…Ower9:7Phiri lopatulika la Asamariya...Yoh 4:20,21

PHIRI LA GILIBOWA (Mount Gilboa)amuna a Israeli anaphedwa pamenepa...1 Sam 31:1Saulo ndi ana ake anaphedwa pamenepa...1 Sam 31:8

PHIRI LA HOREBU (Mount Horeb)ana Aisraeli sanavalenso zokongoletsa pamenepa...Eks 33:6chimodzimodzi ndi Sinai...Eks 3:1

PHIRI LA EBALA (Mount Ebal)lotembereredwa ndi Mulungu...Deut 11:29Yoswa anamanga guwa lansembe pa phiri limeneli...Yos 8:20

PHIRI LA HORO (Mount Hor)Ambuye analankhula kwa Mose ndi Aroni pamenepa...Num20:23Aroni anaferapo...Num 20:25-25

PHIRI (hill)pa Ziyoni phiri langa...Mas 2:6wokhazikika pamwamba pa phiri...Mat 5:14phiri lililonse ndi mtunda...Luk 3:5nanka naye pamutu pa phiri...Luk 4:29

PHIRI LA SINAI (Mount Sinai)Mulungu anatsikirapo, mu moto...Eks 19:18Mulungu anamuitanira Mose pamwamba pake...Eks 19:20ulemelero wa Mulungu unatsikilapo, kwa masiku asanu ndilimodzi...Eks 24:14

PHIRI (mountain)ku phiri la Mulungu...Eks 3:1likagwa phiri, latha...Yob 14:18munakhazikitsa phiri langa...Mas 30:7

Page 134: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

phiri la Basana ndilo phiri...Mas 68:15tikwere kunka kuphiri...Yes 2:3unasanduka phiri lalikulu...Dan 2:35ndiweyani, phiri lalikulu...Zek 4:7mudzati ndi phiri ili...Mat 17:20pamodzi ndi iye m’phiri...2 Pet 1:18sangathe kukwera m’phiri la...Eks 19:23ngati phiri la Karimere...Nyi 7:5akufanizira phiri la Sinai...Agal 4:25

PHOKOSO (clamorous)mkazi wopusa ngwaphokoso...Miy 9:13

PHOKOSO (noise)tamvani phokoso kumapiri...Yes 13:4phokoso lao lilingati...Yes 17:12wa phokoso wataya mwai...Yer 46:17zidzatha ndi phokoso...2 Pet 3:10

PHOMPHO (bottomless)chifunguriro cha dzenje la kuphompho...Chiv 9:1chidzatuluka m’phompho...Chi 17:8chifungulo cha phompho...Chiv 20:1

PHOMPHO (pit)namponya kuphompho, natsekapo...Chiv 20:3[onaninso: chionongeko, dzenje, manda]

PHOPHONYA (excuse)usanene pamaso pa mthenga kuti, ndinaphophonya...Mlal 5:6[onaninso: chowiringula, wiringula]

PHUKA (blossom)Israeli adzaphuka ndi...Yes 27:6ndi kuphuka ngati duwa...Yes 35:1chinkana mkuyu suphuka...Hab 3:17

PHUKIRA (spring)choonadi chiphukira m’dziko...Mas 85:11[onaninso: kasupe, meretsera, oneka]

PHUKITSA (bud)ndikuiphukitsa...Yes 55:10

PHUKUSI (sack)phukusi la ndalama...Gen 42:35

PHULIKA (burst)atsopano akuti aphulike...Yob 32:19naphulika pakati...Mac 1:18[onaninso: phulitsa]

PHULITSA (burst)adzaphulitsa matumba...Luk 5:37[onaninso: phulika]

PHULUSA (ashes)yopanda pake ngati phulusa...Yob 13:12ngati fumbi ndi phulusa...Yob 30:19ndimadya phulusa ngati chakudya...Mas 102:9akuchita ngati kudya phulusa...Yes 44:20nikhala m’mapulusa...Yon 3:6nkuzithira phulusa...Luk 10:13ndiponso phulusa la...Aheb 9:13

PHUNGU (counselor)Wauphungu, Mulungu wamphamvu...Yes 9:6ngakhale mwa iwo palibe phungu...Yes 41:28kapena anakhala phungu...Aro 11:34[onaninso: mfumu]

PHUNZIRA (learn)amve, naphunzire kuopa Yehova...Deut 31:13kuti ndiphunzire malemba...Mas 119:71kuti ungaphunzire mayendedwe ake...Miy 22:25phunzirani kuchita zabwino...Yes 1:17ndipo sadzaphunziranso nkhondo...Yes 2:4goli langa phunzirani kwa ine...Mat 11:29mkazi akhale aphunzire akhale...1 Tim 2:11mu izi zimene waziphunzira...2 Tim 3:14anthu athu aphunzirenso...Tit 3:14

PHUNZIRA (learned)wandipatsa lilime la ophunzira...Yes 50:4inu simunaphunzire Khristu...Aef 4:20pa zonse ndidaphunzira chinsinsi...Afil 4:12anaphunzira kumvera ndi izi...Aheb 5:8[onaninso: phunzitsidwa]

PHUNZIRA (understood)ndaphunzira zambiri zaluntha...Mlal 1:16[onaninso: lingalira, mvetsa, zindikirika]

PHUNZITSA (taught)mwandiphunzitsa kuyambira...Mas 71:17ndani adamphunzitsapo kanthu...Yes 40:13munkaphunzitsa m’miseu...Luk 13:26zimene Atate adandiphunzitsa...Yoh 8:28munthu amene adandiphunzitsa...Agal 1:12[onaninso: phunzitsidwa]

PHUNZITSA (teach)muziwaphunzitsa mwachangu...Deut 6:7ndiwo adzaphunzitse ana...Deut 33:10ndidzakuphunzitsani zimene...1 Sam 12:23angaphunzitse Mulungu nzeru...Yob 21:22ndidzakuphunzitsani zamphamvu...Yob 27:11mundiphunzitse zimene...Yob 34:32mundiphunzitse kuchita kufuna...Mas 25:4mundiphunzitse njira yanu...Mas 27:11dzanja lanu lidzakuphunzitsani zoopsa...Mas 45:4ndidzawaphunzitsa njira zanu...Mas 51:13adzatiphunzitsa njira zake...Yes 2:3ameneyu akuti aphunzitse...Yes 28:9saphunzitsa popanda malipiro...Mika 3:11mumaphunzitsa malamulo...Mat 22:16adzakuphunzitseni zonse...Yoh 14:26sichitiphunzitsa kuti nchamanyazi...1 Akor 11:14mkazi aziphunzitsa kapena...1 Tim 2:12uzilamula ndi kuphunzitsa...1 Tim 4:11uziwaphunzitsa anthu...1 Tim 6:2akuphunzitseninso maphunziro..Aheb 5:12[onaninso: dziwitsa, langiza]

PHUNZITSA (teaches)amaphunzitsa ochimwa...Mas 25:8Mzimu Woyera amatiphunzitsa...1 Akor 2:13munthu wophunzitsa...1 Tim 6:3wina woti akuphunzitseni...1 Yoh 2:27

PHUNZITSA (teaching)muzikawaphunzitsa kusunga...Mat 28:20ankaphunzitsabe ndi kulalika...Mac 5:42ngati ndikuphunzitsa...Akol 1:28pakuwaphunzitsa zimene sayenera...Tit 1:11kumatiphunzitsa kusiyana...Tit 2:12

PHUNZITSIDWA (instructed)anaphunzitsidwa m’njira ya...Mac 18:25utaphunzitsidwa m’chilamulo...Aro 2:18[onaninso: langiza]

Page 135: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

PHUNZITSIDWA (learned)adzakhala onse ophunzitsidwa...Yoh 6:45[onaninso: phunzira]

PHUNZITSIDWA (taught)ophunzitsidwa ndi Mulungu...Yoh 6:45[onaninso: phunzitsa]

PHWANDO (banquet)idakonzera mwana wake phwando...Mat 22:2[onaninso: madyerero]

PHWANDO (feast)Loti adawachitira phwando...Gen 19:3phwando ndi lokondweretsa...Mlal 10:19iwe ukamakonda phwando...Luk 14:13[onaninso: chikondwerero, madyerero]

PHWANYA (break)phwanyani nsagwada...Mas 58:6ngati aphwanya malamulo...Mas 89:31ndipo musachiphwanye...Yer 14:21aphwanya eni mphamvu...Yob 34:24sangathe kuchiphwanya...Agal 3:17munthu angaphwanye pangano...Agal 3:15[onaninso: nyema]

PHWANYA (broken)waphwanya pangano langa...Gen 17:14adaphwanya chipangano chakale...Mas 55:20ndodo ya kabango iyi yophwanyika...Yes 36:6wakugwa pamwala uwu adzaphwanyika...Mat 21:44[onaninso: sweka]

PHWANYA (crush)kuti phazi lingawaphwanye...Yob 39:15adzaphwanya satana pansi...Aro 16:20udzawaphwanya monga mbiya...Mas 2:9Yehova laphwanya mdani...Eks 15:6makanda ao adzatswanyidwe...Yes 13:16ana ao amakanda adzaphwanyika...Hos 13:16

PHWETEKWA (hurt)anthu anga ndaphwetekwa nalo...Yer 8:21[onaninso: chita choipa, chitidwa choipa, pweteka,

pwetekedwa]

PHWETEKWA (suffer)chikole adzaphwetekwapo...Miy 11:15[onaninso: kumva zowawa, zunzidwa]

PIHAHIROTI (Pi Hahiroth)Aisraeli anamanga zithando zao pamenepa asanaoloke nyanjayofiira. Eks 14:2,9; Num 33:7,8

PIKISANA (rebel)ndi amene apikisana nako kuunika...Yob 24:13ndipo sanapikisana nao mau ake...Mas 105:28[onaninso: galukira, panduka, ukira]

PILATO (Pilate)bwanamkubwa wa Yudeya (A.D. 26-36);Luk 3:1anamfunsa Yesu ndi kumpereka kwa Ayuda...Mat27:2,11-26;Yoh 18:28-19:16

PINDA (bent)mpesa uwu unachipindira...Ezek 17:7

PINDA (fold)monga chofunda mudzapinda...Aheb 1:12[onaninso: khola]

PINDULA (profit)mudzapindulanji pa imfa...Mas 30:9munthu amapindulanji ndi...Mlal 1:3munthu angapindulenji atapata...Marko 8:36munthu wapindulanji atapata...Luk 9:25ankapindulitsa mbuye wake...Mac 16:16ataona kuti sangapindulenso...Mac 16:19inkawapindulitsa kwambiri...Mac 19:24Khristu simupindula nayenso...Agal 5:2amatilanga kuti tipindule...Aheb 12:10[onaninso: phindu]

PINDULA (prosper)simudzapindula nazo njira zanu...Deu 28:29chosulidwira iwe chidzapindula...Yes 54:17ipindula njira ya oipa...Yer 12:1monga momwe anapindula...1 Akor 16:2[onaninso: dalitsa, lemera, lemereza, phindu]

PINDULITSA (profitable)zimenezi nzabwino nzopindulitsa...Tit 3:8thupi kumapindulitsapo pang’ono...1 Tim 4:8[onaninso: phindu]

PIRIKITSA (drive)a anthu oipa andipirikitse...Mas 36:11ankawapirikitsa pakati pa anthu...Yob 30:5[onaninso: turutsa]

PIRIKITSA (drove)atampirikitsira kunja Adamuyo...Gen 3:24[onaninso: turutsa]

PIRIRA (endure)anthu akamatizunza timangopirira...1 Akor 4:12motero tsono timapirira...2 Tim 2:10tiwayesa odala opirirawo...Yak 5:11[onaninso: khala chikhalire, khala kosatha]

PIRIRA (endured)atapirira analandira lonjezanolo...Aheb 6:15popeza kuti ankapirira...Aheb 11:27iye amene adapirira udani...Aheb 12:3

PIRIRA (endures)wakupirira kufikira chimaliziro...Mat 10:22chipirira zinthu zonse...1 Akor 13:7wodala munthu wakupirira...Yak 1:12[onaninso: khala chikhalire]

PIRIRA (patient)pirirani m’masautso...Aro 12:12[onaninso: leza mtima]

PISIDIYA ( Pisidia)Paulo anayenderako kawiri...Mac 13:13,14;14:24

PISIGA (Pisgah)Balamu anaperekerapo nsembe...Num 23:14Mose anaona dziko la malonjezo pamenepa...Deut 3:27Malo omwe Mose anafera...Deut 34:1-7

PISONI (Pishon)umodzi mwa mitsinje inayi ya mu Edeni...Gen 2:10,11

PITA (go)leke ndidzipita chifukwa kuli kucha...Gen 32:26uwalole anthu anga apite...Eks 5:1mukapanda kupita nafe limodzi...Eks 33:15kumene mupite inuko inenso ndipita...Rut 1:16taonani ndikapita chakutsogolo...Yob 23:8pakuti ndidapita ndi unyinji...Mas 42:4

Page 136: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndidzapita kuti pofuna kupewa...Mas 139:7pita kwa nyerere mlesi iwe...Miy 6:6zonse zimapita kumodzimodzi...Mlal 3:20kulibwino kupita kunyumba...Mlal 7:2ndidzikutsatani kulikonse kumene mudzipita...Mat 8:19ali kuchipululu, musadzapiteko...Mat 24:26pitani kudziko lonse...Marko 16:15ndikauza wina kuti pita...Luk 7:8nanga tingapitenso kwa yani...Yoh 6:68adawauza kuti, “Ine ndikupita...Yoh 8:21ndikupita kukakukonzerani inu malo...Yoh 14:2chifukwa ndikupita kwa Atate...Yoh 14:12mukufuna ine, awa alekeni apite...Yoh 18:8[onaninso: tsikira]

PITA (pass)ndipo ndidzakupititsani pansi...Ezek 20:37[onaninso: dutsa, pitirira]

PITA (passed)Yehova anapitapo...1 Maf 19:11[onaninso: pyoza]

PITA (passes)mphepo ikapitapo pakhala...Mas 103:16[onaninso: posa]

PITIKITSA (chase)anthu asanu okha mwa inu adzapitikitsa...Lev 26:8modzi akadapitikitsa zikwi...Deut 32:30ndipo mngelo wa Yehova awapitikitse...Mas 35:5

PITIRIRA (beyond)musapitirire zimene malembo akunena...1 Akor 4:6ngakhalenso mopitirira pamenepo...Aheb 12:24[onaninso: posa]

PITIRIRA (pass)magaziwo, ndidzakupitirirani...Eks 12:13[onaninso: dutsa, pita]

PITOMU (Pithom)mzinda wa ku Ejipito womangidwa ndi akapolo a chiyuda...Eks1:11

POGONA (bed)ndikayala pogona panga mumdima...Yob 17:13pogona pathu mpa msipu...Nyim 1:16ndi pogona pakhale posadetsedwa...Aheb 13:4[onaninso: kama, mphasa, tchika]

POKHALA (habitation)yakunka pokhala panu poyera...Eks 15:13pokhala pako polungama...Yob 8:6mokhala mwake mmoyera...Mas 68:5pokhala pao pakhale bwinja...Mas 69:25ku mudzi wokhalamo...Mas 107:7mudzi wokhalamo...Mas 107:36adalitsa mokhalamo olungama...Miy 3:33ndi mokhala okhulupirika...Yes 32:18mokhalira mwake mopatulika...Zek 2:13kuvekedwa ndi chokhalamo...2 Akor 5:2

PONDA (trample)udzatha kuponda mkango...Mas 91:13muzipondaponda m’mabwalo...Yes 1:12mphamvu kuti muziponda njoka...Luk 10:19[onaninso: pondereza]

PONDA (trampled)anamuponda kunja kwa mudzi...Chiv 14:20[onaninso: pondereza, ponderezedwa]

PONDA (tread)udzatha kuponda mkango...Mas 91:13ngati anthu aponda mphesa...Yer 25:30nadzaponda pa misanje...Mika 1:3za munthu woponda mphesa...Yes 63:2[onaninso: pondereza]

PONDA (treads)waponda mopondera mphesa...Yes 63:2naponda pamisanje ya dziko...Amo 4:13ndipo aponda Iye moponderamo...Chiv 19:15[onaninso: puntha]

PONDEREZA (oppresses)wopondereza m’mphawi...Miy 14:31amene amapondereza osauka...Miy 22:16amene amapondereza osauka...Miy 28:3

PONDEREZA (trample)mphamvu zanu tidzapondereza...Mas 44:5mudzapondereza anthu oipa...Mal 4:3kuopa kuti zingazipondereze...Mat 7:6[onaninso: ponda]

PONDEREZA (trampled)ndapondereza ndekha anthu...Yes 63:3mudapondereza anthu a...Hab 3:12akunja adzampondereza...Luk 21:24iye amene anapondereza Mwana...Aheb 10:29[onaninso: ponda, ponderezedwa]

PONDEREZA (tread)oipa onse uwapondereze...Yob 40:12amene adzapondereza adani...Mas 60:12iwowo adzaupondereza mzinda...Chiv 11:2[onaninso: ponda]

PONDEREZEDWA (trampled)adzaponderezedwa ngati matope...Mik 7:10[onaninso: ponda, pondereza]

PONTO (Pontus)Ayuda ochokera kumeneku analipo patsiku la Pentekoste...Mac2:5,9kwawo kwa Akwila...Mac 18:2Akhristu ochokera kumeneku analankhulidwa ndi Petro...1 Pet1:1

PONYA (threw)namponya mdzenje la mikango...Dan 6:16ndipo aponya pansi akorona...Chiv 4:10analikuponya psasa m’nyanja...Mat 4:18[onaninso: ponyedwa]

PONYEDWA (threw)losaponyedwa thupi lako lonse...Mat 5:29ndipo chinaponyedwa pansi...Chiv 12:9[onaninso: ponya]

PORKIO FESITO (Porcius Festus)Paulo anaima pa mlandu pamaso pake...Mac 25:1-22

POSA (above)wophunzira saposa mphunzitsi wake...Mat 10:24[onaninso: kumwamba, m’mwamba, pamwamba]

POSA (abundantly)Iye amene angathe kuchita koposaposatu zonse zimene...Aef

3:20[onaninso: chuluka, zonona]

Page 137: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

POSA (better)kokoma kuposa nsembe...1 Sam 15:22koposa kukhulupirira munthu...Mas 118:8iposa nyumba yodzala nyama...Miy 17:1aposa wokhetsa milomo...Miy 19:1kuposa kukhala ndi mkazi...Miy 21:19mnansi wapafupi aposa mbale...Miy 27:10lodzala pali mtendere liposa...Mlal 4:6awiri aposa mmodzi...Mlal 6:9mbiri yabwino iposa zonunkhira zabwino...Mlal 7:1adaposa anyamata onse...Dan 1:20atakhala wakuposa angelo...Aheb 1:4kuti za inu zili zoposa...Aheb 6:9chokoma choposa...Aheb 12:24[onaninso: pambana]

POSA (beyond)koposa mphamvu yao...2 Akor 8:3ndinalondalonda Mpingo wa Mulungu koposa...Agal 1:14[onaninso: pitirira]

POSA (exceeds)kukhulupirika kwanu sikuposa...Mat 5:20lina liposa linzake...Aro 14:5saposa mphunzitsi...Mat 10:24limene liposa...Afil 2:9

POSA (greater)wakuposa kachisiyo ali pomapano...Mat 12:6wakuposa Yona ali pompano...Mat 12:41wakuposa Solomo ali pompano...Mat 12:42udzaona zoposa izi...Yoh 1:50ali nacho chikondi choposa...Yoh 15:13chokometsera choposa...1 Akor 12:23ndipo wakunenera aposa...1 Akor 14:5umboni wa Mulungu uposa...1 Yoh 5:9[onaninso: wamkulu]

POSA (passes)chakuposa mazindikiridwe...Aef 3:19[onaninso: pita]

POTIFARA (Potipher)nduna yaikulu ya ku Ejipito...Gen 39:1anamuika Yosefe mndende...Gen 39:20

POTIFERA (Potipherah)wansembe wa ku Ejipito...Gen 41:45-50atate ake a Asenati, mkazi wake wa Yosefe...Gen 46:20

POTSEGULIRA (entrance)potsegulira mau anu...Mas 119:130[onaninso: khomo lolowera]

PRISILA (Priscilla)mkazi wa Akwila...Mac 18:1-3limodzi ndi Akwila anamulangiza Apolo...Mac 18:26ananenedwa ndi Paulo...Aro 16:3;1 Akor 16:19;2 Tim 4:19

PROKORO (Prochorus)mmodzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:5

PSEREZA (burning)muli moto wopsereza...Miy 16:27

[onaninso: tentha]

PSEREZA (burnt)nsembe yopsereza...Gen 22:7nsembe yopsereza simuikonda...Mas 51:16nsembe zopsereza zanu...Yer 6:20nsembe zanu zopsereza...Amo 5:22

PSINJIKA (distress)simudzakhala popsinjika...Yob 36:19kapena kupsinjika mtima...Aro 8:35[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, nsautso, opsa,saukira, sautsika]

PUBLIO (Publius)mkulu wachiroma, anamlandira Paulo...Mac 28:7

PULO (Pul)mfumu ya ku Asiriya, dzina lakenso ndi Tigilati Pilaza...2 Maf15:19— dziko ndi anthu ku Africa...Yes 66:19

PULUMUKA (escape)wolankhula mabodza sadzapulumuka...Miy 19:5ife tinathawira atithangate kupulumutsidwa...Yes 20:6mphamvu zopulumukira ku zonsezi...Luk 21:36kuti udzapulumuka pa mlandu...Aro 2:3adzakukonzera njira yopulumukira...1 Akor 10:13tingapulumuke bwanji tikapanda...Aheb 2:3sadapulumuke ku chilango ai...Aheb 12:25[onaninso: pulumutsidwa, thawa]

PULUMUKA (escaped)wapulumukira pang’onong’ono...Yob 19:20ndipo ife tapulumuka...Mas 124:7anthu apulumuka kuzodetsa...2 Pet 2:20

PULUMUKA (saved)chapita, koma sitidapulumukebe...Yer 8:20nanga angathe kupulumuka...Mat 19:25chiyani kuti ndipulumuke...Mac 16:30chakuti Aisraeli apulumuke...Aro 10:1Aisraeli onse adzapulumuka...Aro 11:26anthu amene akupulumuka...2 Akor 2:15anthu onse apulumuke...1 Tim 2:4mkazi adzapulumukabe...1 Tim 2:15adapulumuka ndi madzi...1 Pet 3:20[onaninso: pulumutsa]

PULUMUTSA (deliver)adzakupulumutsa m’masautso...Yob 5:19wakupulumutsa m’dzanja lanu...Yob 10:7nzeru idzakupulumutsa...Miy 2:16sudzapulumutsa akuzolowerana...Mlal 8:8mutipulumutse kwa oipayo...Mat 6:13iye ampulumutse tsopano...Mat 27:43adziwa kupulumutsa opembedza...2 Pet 2:9[onaninso: landitsa, ombola]

PULUMUTSA (delivered)pakuti ndinapulumutsa wozunzika...Yob 29:12Yesu wotipulumutsa ife...1 Ates 1:10[onaninso: landitsa, perekedwa]

PULUMUTSA (save)Chauta sapulumutsa anthu...1 Sam 17:47koma amapulumutsa odzichepetsa...2 Sam 22:42adzapulumutsa wodzichepetsayo...Yob 22:29mudzandilanditse, mudzandipulumutse...Mas 6:4pulumutsani anthu anu...Mas 28:9kumwamba ndipo adzandipulumutsa...Mas 57:3adzapulumutsa ana aumphawi...Mas 72:4adzapulumutsa anthu osowa...Mas 72:13yembekeza Yehova adzakupulumutsa...Miy 20:22akubwera kudzakupulumutsa...Yes 35:4Chauta wandipulumutsa...Yes 38:20ndipo ndidzapulumutsa ana ako...Yes 49:25kuti angalephere kukupulumutsani...Yes 59:1wa mphamvu yakupulumutsa...Yes 63:1sangathenso kupulumutsa anthu...Yer 14:9

Page 138: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndidzakulanditsa ndi kukupulumutsa...Yer 15:20pulumutseni ndipo ndidzapulumukadi...Yer 17:14Chauta wakupulumutsa anthu...Yer 31:7kuti ikupulumutse m’midzi yako...Hos 13:10Asiriya sadzatipulumutsa...Hos 14:3wamphamvu wakupulumutsa...Zef 3:17adzapulumutsa anthu ake...Mat 1:21wofuna kupulumutsa moyo wake...Mat 16:25adabwera kudzapulumutsa...Mat 18:11kupulumutsa moyo wa munthu...Marko 3:4adzipulumutse yekha ngati...Luk 23:35udzipulumutse wekha ndi ife...Luk 23:39mundipulumutse ku nthawi...Yoh 12:27mlandu koma kudzawapulumutsa...Yoh 12:47ndi kupulumutsa ena mwa iwo...Aro 11:14ku dziko lapansi kupulumutsa ochimwa...1 Tim 1:15adzapulumutsa anthu ochimwa...1 Tim 4:16ndiwo angathe kukupulumutsani...Yak 1:21chikhulupiriro chotere chingampulumutse...Yak 2:14

PULUMUTSA (saved)umene Chauta adaupulumutsa...Deut 33:29adapulumutsa anthu ena...Mat 27:42adzatipulumutsa kwa adani...Luk 1:71chanu chakupulumutsani...Luk 7:50koma kuti adzawapulumutse...Yoh 3:17Mulungu adatipulumutsa...Aro 8:24mzimu wake udzapulumutsidwe...1 Akor 5:5Mulungu adzakupulumutsani...1 Akor 15:2kumene kudakupulumutsani...Aef 2:8choncho adatipulumutsa...Tit 3:5[onaninso: pulumuka]

PULUMUTSA (saves)amapulumutsa osauka...Yob 5:15amapulumutsa otaya mtima...Mas 34:18masiku ano umakupulumutsani...1 Pet 3:21

PULUMUTSA (saviour)wachilungamo ndi wopulumutsa...Yes 45:21motere ndi wopulumutsa...Yes 63:8[onaninso: mpulumutsi]

PULUMUTSA (well)chikhulupiriro chako chakupulumutsa...Marko 5:34[onaninso: chitsime, bwino,koma, komera, limba, ngwiro]

PULUMUTSIDWA (escape)ife tinathawira atithangate kupulumutsidwa...Yes 20:6[onaninso: pulumuka, thawa]

PUMA (breath)analeka kupuma...1 Maf 17:17iwo akupumira zachiwawa...Mas 27:12zonse zakupuma...Mas 150:6[onaninso: mpweya]

PUMULA (ease)upumule, uzidya...Luk 12:19[onaninso: kukhala mosavuta, mtendere]

PUNDUKA (maimed)kulowa m’moyo wopunduka...Marko 9:43muno aumphawi ndi opunduka...Luk 14:21

PUNTHA (beat)nyamuka nupunthe mwana wamkazi...Mika 4:13[onaninso: guguda, menya, panda]

PUNTHA (treads)ng’ombe yopuntha tirigu...1 Tim 5:18[onaninso: ponda]

PURIMU (Purim)amawatcha kuti masiku a Purimu...Ester 9:26

PWETEKA (hurt)nkupweteka mai wa pathupi...Eks 21:22koma sadandipweteke...Miy 23:35nthawi yakuti wina apweteka mnzake...Mlal 8:9sipadzakhala chilichonse chopweteka...Yes 11:9chifukwa cha kupweteka...Yer 10:19[onaninso: chita choipa, chitidwa choipa, phwetekwa,pwetekedwa]

PWETEKEDWA (hurt)chotha kuwapha, sadzapwetekedwa...Marko 16:18[onaninso: chita choipa, chitidwa choipa, phwetekwa,

pweteka]

PYOZA (passed)wopyoza miyamba...Aheb 4:14[onaninso: pita]

R

RABA (Rabbah)mzinda waukulu wa Amoni...Amo 1:14unagonjetsedwa ndi Yowabu; unatengedwa ukapolo ndiDavide...2 Sam 12:26-31chionongeko chake chinanenedweratu...Yer 49:2

RABONI (Rabboni)Mariya anamutcha Yesu dzina limeneli...Yoh 20:16

RAHABU (Rahab)mkazi wadama wa ku Yeriko; anathandiza azondi aYoswa...Yos 2:1-21sanaphedwe nthawi ya nkhondo...Yos 6:17-25ananenedwa m’Chipangano Chatsopano...Mat 1:5;Aheb11:31;Yak 2:25— anagwiritsidwa ntchito ponenera za Ejipito...Mas 87:4

RAKELE (Rachael)mwana wamkazi wamng’ono wa Labani;mkazi wokondedwa kwambiri kwa Yakobo...Gen 29:28-30anathandizira udindo wa mwamuna wake...Gen 31:14-16make a Yosefe ndi Benjamini...Gen 30:22-25uneneri wake unalembedwanso...Yer 31:15; Mat 2:18

RAMA (Ramah)anamangira linga...1 Maf 15:17-22likulu la Samuele...1 Sam 7:15,17Davide anathawirako...1 Sam 19:18-23

RAMOTI MGILIYADI ( Ramoth in Gilead)mzinda wothawirako kummawa kwa Yordane...Deut4:43;Yosw 20:8; 1 Mbir 6:80pamene Ahabu analimbana ndi Asiriy...1 Maf 22:1-39

RAMESE (Raamses)mzinda wosungiramo chakudya womangidwa ndi Ayuda...Eks1:11

REBEKA (Rebecca)ali mu mndandanda wa zizukulu za Abrahamu...Gen 22:20-23anakhala mkazi wake wa Isaki...Gen 24:15-67mai ake a Yakobo ndi Esau...Gen 25:21-28anamulimbikitsa Yakobo kuti ampusitse Isaki kenakankuthawa...Gen 27:1-29,42-46

REZINI (Rezin)Mfumu ya ku Damasiko; inagwirizana ndi Peka kukulimbanandi Ahazi...2 Maf 15:37zomwe anachita zinapangitsa Yesaya kulosera za Mesiya...Yes

Page 139: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

7:1-9:12

REZONI (Rezon)Mwana wa Eliyada, anakhazikitsa ufumu wa Siriya...1 Maf11:23-25

RIBILA (Riblah)likulu la:Farao Neko...2 Maf 23:31-35Nebukadinezara...2 Maf 25:6,20,21Zedekiya anachititsidwa khungu pamenepa...Yer 39:5-7

RIZIPA (Rizpah)mzakazi wa Saulo yemwe anatengedwa ndi Abineri...2 Sam3:6-8ana ake anaphedwa...2 Sam 21:8,9anagwidwa ndi chisoni, nayamba kusamala mitembo...2 Sam21:10-14

RODA (Rhoda)mzikazi...Mac 12:13-16

ROMA (Rome)Ayuda anachotsedwako...Mac 18:2Paulo analembera akhristu ake...Aro 1:7Paulo anakhumba kupitako...Mac 19:21Paulo anapitako...Mac 28:14Paulo anamangidwako...Mac 28:16

RUBENI (Reuben)mwana wamkulu wa Yakobo...Gen 29:31,32anagona ndi Biliha, anataya ulemu wake...Gen 35:22; 49:3,4anakonza zompulumutsa Yosefe...Gen 37:21-30analonjeza kupereka ana ake chifukwa cha Benjamini...Gen42:37— fuko lake: linawerengedwa...Num 1:20,21,26:5-11anakhala kumawa kwa Yordane...Num 32:1-42analowelera nkhondo kumenyana ndi Akenani...Yos 1:12-18Anamanga guwa la nsembe la Chikumbutso...Yos 22:10-34

RUTE (Ruth)M’mowabu...Rut 1:4anatsatira Naomi...Rut 1:6-18anakwatiwa ndi Bowazi...Rut 4:9-13kholo la makolo a Khristu...Rut 4:13,21,22

S

SABATA (Sabath)lopuma, tsiku la sabata...Eks 16:23uzikumbukira tsiku la sabata...Eks 20:8masiku a sabata...Ezek 20:12adaika tsiku la sabata...Marko 2:27mwezi ndi za sabata...Yoh 5:18

SADRAKE (Shadrack)dzina la Hananiya la ku Babulo...Dan 1:3,7anaponyedwa m’ng’anjo ya moto...Dan 3:1-28

SAFANI (Shaphan)mphunzitsi wa malamulo pansi pa Yosiya...2 Maf 22:3-14

SAFIRA (Saphira)mkazi wa Ananiya; anakanthidwa chifukwa chonama...Mac5:1-11

SAKA (hunt)choipa chidzamsaka munthu wachiwawa...Mas 140:11[onaninso: funafuna]

SALEMU (Salem)dzina loyambirira la Yerusalemu...Gen 14:18

limagwiritsidwa ntchito mndakatulo...Mas 76:2

SALIMANEZERE (Shalmanezer)mfumu ya Asiriya...2 Maf 17:3

SALIMO (Psalm)mudalembedwera msalimo lachiwiri...Mac 13:33yense ali nalo salimo...1 Akor 14:26[onaninso: zomlemekeza]

SALOME (Salome)mmodzi wa atumiki otumikira achizimayi...Marko 15:40,41anapita kumanda opanda kanthu..Mark 16:1— mwana wamkazi wa Herodiya (sanatchulidwe dzina lakem’Baibulo)...Mat 14:6-11

SALUMU (Shallum)mfumu ya Israel...2 Maf 15:10-15

SAMA (Shammah)mwana wa Yese...1 Sam 16:9wotchedwa Simea...1 Mbir 2:13— mmodzi wa amuna amphamvu a Davide...2 Sam 23:11wotchedwanso Samoti-hori...1 Mbir 11:27

SAMALA (care)Ambuye, kodi simusamalako...Luk 10:40amene ali ndi mtima wosamala...Afil 2:20Iye ndiye amakusamalirani...1 Pet 5:7chifukwa anali kusamalira osauka...Yoh 12:6palibe wina wosamalira moyo wanga...Mas 142:4[onaninso: nkhawa]

SAMALA (cares)palibe mmodzi wosamala...Mas 142:4[onaninso: nkhawa]

SAMALA (cherishes)koma amalidyetsa ndi kulisamala...Aef 5:29ngati mai osamalira ana ake...1 Ates 2:7

SAMALIRA (attention)usamalire kuwerenga...1 Tim 4:13[onaninso: mvetsa, penyerera]

SAMARIYA (Samaria)likulu la Israeli...1 Maf 16:24-29unagonjetsedwa ndi Beni-Hadadi...1 Maf 20:1-21unagonjetsedwanso, napulumutsidwa modabwitsa...2 Maf6:24-7:20anthu okhala kumeneko anagwidwa ndi Aasiriya;anadzazidwa ndi anthu achikunja...2 Maf 17:5,6,24-41— boma la Pelestina nthawi ya Khristu...Luk 17:11-19ophunzira adalesedwa kulalikirako...Mat 10:5uthenga wabwino unalalikirako pamene Yesu anakwerakumwamba...Mac 1:8;9:31;15:3

SAMBA (bathed)amene anatha kusamba...Yoh 13:10

SAMBA (wash)ngakhale ndisambe thupi...Yob 9:30ndimasamba m’manja...Mas 26:6adzasamba mapazi ake...Mas 58:10sambani dziyeretseni...Yes 1:16samba m’maso nkudzola...Mat 6:17sasamba manja pakudya...Mat 15:2sasamba m’manja...Marko 7:3 “pita ukasambe kudziwe...Yoh 9:7[onaninso: sambitsa, sambitsidwa, tsuka]

SAMBA (washed)

Page 140: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndasamba m’manja...Mas 73:3nkusamba m’manja...Mat 27:24[onaninso: chapa, konkha, masula, sambitsa, sambitsidwa,

tsuka]

SAMBITSA (wash)mundisambitse kwathunthu...Mas 51:2madzi akusambitsa mapazi anga...Luk 7:44nayamba kusambitsa mapazi...Yoh 13:5ngati sindikusambitsa...Yoh 13:8muyenera kumasambitsana...Yoh 13:14[onaninso: samba, sambitsidwa, tsuka]

SAMBITSA (washed)adzakhala atasambitsa...Yes 4:4sadakusambitse m’madzi...Ezek 16:4atatha Iye kusambitsa mapazi...Yoh 13:12ankasambitsa mapazi...1 Tim 5:10[onaninso: chapa, konkha, masula, sambitsidwa, tsuka]

SAMBITSIDWA (wash)ubatizidwe ndi kusambitsidwa...Mac 22:16[onaninso: samba, sambitsa, tsuka]

SAMBITSIDWA (washed)koma munasambitsidwa...1 Akor 6:11[onaninso: chapa, konkha, masula, sambitsa, tsuka]

SAMIGARA (Shamgar)oweruza wa Israeli amene anapha Afilisti 600...Ower 3:31

SAMIRA (lay)alibe posamira mutu wake...Mat 8:20[onaninso: ika, vula]

SAMISONI (Samson)kubadwa kwake kunaloseredwa ndipokunakwaniritsidwa...Ower 13:2-25anakwatira mkazi wachifilisti; abwezera kuperekedwakwake...Ower 14anagonjetsa Afilisti, mmodzimmodzi...Ower 15anaperekedwa ndi Delila...Ower 16:4-22anapha anthu ambiri pa imfa yake...Ower 16:4-22

SAMUELE (Samuel)kubadwa kwake kunali yankho; anaperekedwa kwaMulungu...1 Sam 1:1-28analandira vumbulutso, anasankhidwa kukhala mneneri...1Sam 3:1-21anaweruza Israeli...1 Sam 7:15-17anachenjeza Israeli za mfumu...1 Sam 8:10-18anadzoza Saulo...1 Sam 9:15-10:1anadzudzula Saulo...1 Sam 15:10-35anadzoza Davide...1 Sam 16:1-13imfa yake...1 Sam 25:1

SANDULIKA (altered)nkhope yake anasandulika...Luk 9:29komabe tonse tidzasandulika...1 Akor 15:51

SANDUTSA (exchanged)anasandutsa choonadi cha...Aro 1:25anasandutsa machitidwe ao...Aro 1:26[onaninso: sinthana]

SANGALALA (enjoy)kuti tisangalale nazo...1 Tim 6:17[onaninso: kondwera]

SANGALATSA (comfort)kumlilira ndi kumsangalatsa...Yob 2:11ndi ndodo yanu izi zindisangalatsa...Mas 23:4

Yehova adzasangalatsanso Ziyoni...Zek 1:17iye asangalatsidwa pano...Luk 16:25[onaninso: tonthoza]

SANIBALATI (Sanballat)msamariya; anayesa kusokoneza zolinga za Nehemiya...Neh2:10; 4:7,8; 6:1-14

SANKHA (appoint)amene anandisankha Ine...2 Sam 6:21[onaninso: ika]

SANKHA (choose)tsono sankhani moyo...Deut 30:19usasankhe njira yake...Miy 3:31kukana choipa ndi kusankha...Yes 7:15ndipo adzasankhanso Israeli...Yes 14:1nadzasankhamo Yerusalemu...Zek 1:17inu simunandisankha ine...Yoh 15:16sindizindikiranso chimene ndidzasankha...Afil 1:22adzamlangiza iye njira adzasankheyo...Mas 25:12poyamba Mulungu anasankha mwa inu...Mac 15:7monga anatisankha ife...Aef 1:4Mulungu anakusankhani inu...2 Ates 2:13

SANKHA (chosen)inu ana a Yakobo, osankhika ake...1 Mbir 16:13anthu amene Chauta wawasankha...Mas 33:12ndinasankha njira yokhulupirika...Mas 119:30ndi mtumiki wanga amene ndakusankha...Yes 43:10pakuti Mariya adasankha dera lokoma...Luk 10:42ndidziwa amene ndawasankha...Yoh 13:18Mulungu wa makolo athu anakusankhiratu...Mac 22:14kodi Mulungu sanasankha osauka...Yak 2:5[onaninso: sankhidwa, sankhula]

SANKHA (elect)amene Mulungu adawasankha...Aro 11:7Mulungu Atate adakusankhani...1 Pet 1:2ndasankha mwala wamtengo...1 Pet 2:6anakuitanani ndipo anakusankhani...2 Pet 1:10[onaninso: sankhidwa]

SANKHA (exalt)ndikapanda kusankha Yerusalemu...Mas 137:6[onaninso: kweza, lemekeza, sankha]

SANKHIDWA (chosen)ndachita chipangano ndi wosankhidwa wanga...Mas 89:3ndinu mbadwa yosankhidwa...1 Pet 2:9[onaninso: sankha, sankhula]

SANKHIDWA (elect)chifukwa cha wosankhidwa wanga...Yes 45:4anthu anga osankhidwa...Yes 65:22kuti akasonkhanitse osankhidwa...Mat 24:31mbale wanu wosankhidwa...2 Yoh 13[onaninso: sankha]

SANKHIKA (acceptable)kukalalika chaka chosankhika...Luk 4:19[onaninso: komera, kondweretsa, landiridwa, landirika]

SANKHULA (chosen)koma Mulungu anasankhula zopusa za dziko lapansi...1 Akor1:27[onaninso: sankha, sankhidwa]

SANKHULA (uphold)kapena kugwirizitsa ochita...Yob 8:20mundichirikize monga mwa mau...Mas 119:116amene ndamsankhula...Yes 42:1

Page 141: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndinadabwa kuti panalibe wochirikiza...Yes 63:5[onaninso: chirikiza, gwirizitsa]

SANTHULA (inquire)ichi anafunafuna nasanthula aneneri...1 Pet 1:10[onaninso: funsira]

SANZA (vomit)monga linasanza mtundu wa anthu...Lev 18:28[onaninso: masanzi]

SARA/SARAI (Sarah/Sarai)mkazi wouma wa Abrahamu...Gen 11:29-31ananenedwa kukhala mlongo wake wa Abramu...Gen12:10-20anampatsa Abramu mdzakazi wake kuti agone naye...Gen16:1-3analandira lonjezo la mwana wamwamuna...Gen 17:15-21anabala Isaki...Gen 21:1-8

SARDI (Sardis)amodzi a malo a mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 1:11

SARONI (Sharon)malo a thyathyathya pakati pa Yopa ndi phiri la Karimero...1Mbir 27:29otchuka ndi maluwa okongola...Nyi 2:1anthu okhalamo, anatembenukira kwa Ambuye...Mac 9:35

SATANA (satan)satana adafuna kuvititsa...1 Mbir 21:11nayenso satana adafika...Yob 1:6adauza satana kuti...Zek 3:2mchipululu kuti satana akamuyese...Mat 4:1choka! Satana...Mat 4:10choka apa iwe satana...Mat 16:23umene Mulungu anakonzera satana...Mat 25:41mu ufumu wa satana...Marko 3:23kumeneko satana ankamuyesa...Luk 4:2satana amabwera nkuchosa...Luk 8:12satana ali kugwa...Luk 10:18satana kuti akupeteni...Luk 22:31mmodzi mwa inu ndi satana...Yoh 6:70inu ndinu ana a satana...Yoh 8:44satana nkuti atayika kale...Yoh 13:2kugwidwa ndi satana...Mac 5:3musampatse mpata satana...Aef 4:27polimbana ndi ndale za satana...Aef 6:11mumpereke kwa satana...1 Akor 5:5satana yemwe amazizimbaitsa...2 Akor 11:4ndi mphamvu za satana...2 Ates 2:9adzapulumuka mumsampha wa satana...2 Tim 2:26satana muzilimbana naye ndipo...Yak 4:7amachimwa, ndi wa satana...1 Yoh 3:8pamene iye ankakangana ndi satana...Yuda 9mpingo wa satana...Chiv 2:9satana adzakuponyetsani mndende...Chiv 2:10wachifumu wa satana...Chiv 2:13zinsinsi zozama za satana...Chiv 2:24mdiyerekezi ndiponso satana...Chiv 12:9adzamtulutsa satanayo...Chiv 20:7

SAUKA MUMZIMU (grieved)wakusiyidwa ndi wosauka m’mzimu...Yes 54:6[onaninso: lira misonzi, mvetsa chisoni]

SAUKIRA (distress)muchoke posaukira...Yob 36:16[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, nsautso, opsa,psinjika, sautsika]

SAULO (Saul)

anakhala mfumu yoyamba ya Israeli...1 Sam 9—11anapereka nsembe mosayenera...1 Sam 13:1-14anamenya nkhondo ndi Afilisti...1 Sam 13:15—14:52sanamvere lamulo la Mulungu anakanidwa ndi Mulungu...1Sam 15anavutika ndi mizimu yoipa...1 Sam 16:14-23anayamba kumchitira nsanje Davide; anayesa kumupha...1Sam 18:5—19:22anatsatira Davide; kawiri konse kamene Davide anamusiyaosamupha...1 Sam 22-24;26anakafunsira kwa woombedza...1 Sam 28:7-25anagonjetsedwa, anadzipha, wakwiriridwa...1 Sam 31—wa ku Tarsa; mtumwi wa amitundu;onani Paulo

SAUTSA (afflict)pakutero awasautse ndi...Eks 1:11Mulungu adzamva, nadzawasautsa...Mas 55:1ndi kusautsa...Yer 31:28samasautsa dala...Mali 3:33[onaninso: vutitsa, zunza, zunzika]

SAUTSA (afflicted)pamene Mphambe wandisautsa...Rut 1:21mudasautsa mitundu ina...Mas 44:2anandisautsa kawirikawiri...Mas 129:1anapirira masautso athu...Yes 53:3anthu adamsautsa...Yes 53:7[onaninso: sautsidwa, osauka, zunzika]

SAUTSA (cheat)usamasautsa mnansi wako...Lev 19:13[onaninso: kulanda, nyenga]

SAUTSIDWA (afflicted)iwe wasautsidwa...Yes 54:11anamwali ake asautsidwa...Mali 1:4wothandiza wosautsidwa...1 Tim 5:10osowa, osautsidwa...Aheb 11:37[onaninso: sautsa,sautsidwa, osauka, zunzika]

SAUTSIKA (distress)m’mene ndinasautsika...Mas 118:5[onaninso: chisauko, chivuto, mavuto, nsauko, nsautso, opsa,psinjika, saukira]

SEALATIELE (Shealtiel)mwana wa mfumu Yekoniya ndiponso tate wa Zerubabele...1Mbir 3:17

SEARI-YASUBU (Shear-Jashub)dzina lokhala ndi tanthauzo lopatsidwa kwa mwana waYesaya...Yes 7:3

SEBA (Sheba)dziko lake linadzadza ndi Asabe wotchuka ndi kuchitamalonda...Yob 1:15; Mas 72:10mfumukazi yake inachezera Solomoni ndipo anadabwa ndinzeru zake...1 Maf 10:1-13ananenedwa ndi Khristu...Mat 12:42

SEBINA (Shebna)msungichuma nthawi ya Hezekiya...Yes 22:15anatsitsidwa kufika pa mphunzitsi wa malamulo...2 Maf 19:2munthu wodzikuza ndi wachuma; mmalo mwake munalowaEliyakimu...Yes 22:19-21

SEFUKIRA (abundance)malingaliro a mitima yao asefukira...Mas 73:7[onaninso: chuluka, chuma, mphamvu, ukulu, yambiri,

zonona]

SEIRI (Seir)

Page 142: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kwao kwa Esau...Gen 32:3Ahori akumeneko anachotsedwa ndi zidzukulu za Esau...Deut2:12kuonongedwa kwake...Ezek 35:15

SEKEMU (Shechem)mwana wa Hamori; anamgwiririra Dina, mwana wamkazi waYakobo...Gen 34:1-31— mzinda wakale wa Efraimu...Gen 33:18mau otsanzikana a Yoswa anaperekedwa pamenepa...Yos24:1-25anamthandiza Abimeleki; anawonongedwa...Ower 9anamangidwanso ndi Yeroboamu...1 Maf 12:25

SEKERETSA (delight)ochita ntheradi amsekeretsa...Miy 12:22[onaninso: chikondwerero, kondwera, kwezeka]

SEMAYA (Shemaiah)mneneri wa Yuda...1 Maf 12:22-24anafotokoza za kugonjetsedwa kwa Sisaki kukhala chilangocha kwa Mulungu..2 Mbir12:5-8analemba za ulamuliro wa Rehoboamu...2 Mbir 12:15

SEMERI (Shemer)anamgulitsa Omuri phiri pomwe Samariya anamangidwapo...1Maf 16:23,24

SEMU (Shem)mwana wamkulu wa Nowa...Gen 5:32anapulumuka chigumula...Gen 7:13analandira mdalitso...Gen 9:23,26kholo la a Semi...Gen 10:22-32

SENAKERIBU (Sennacherib)mfumu ya ku Asiriya (705-681B.C.)mwana ndi wolowa m’malo mwa Sargoni wachiwiri...2 Maf18:13imfa yake anachita chophedwa...2 Maf 19:36,37

SENDERA (approach) asasendere wina wa inu...Lev 18:6[onaninso: yandikira]

SENZA (attend)ndidzakusenzani inu kuipa kwa ntchito zanu...Yer 23:2[onaninso: imva]

SENZA (bore)amene anasenza machimo athu mwini yekha...1 Pet 2:24[onaninso: bala, bereka, nyamula]

SENZA (carry)amene aliyense sasenza...Luk 14:27kusenza machimo a ambiri...Aheb 9:28ndipo anasenza mtanda yekha...Yoh 19:17osenza thonzo lake...Aheb 13:13[onaninso: nyamula, tenga]

SERAFI (seraphim)padaimirira aserafi...Yes 6:2

SERGIO PAULO (Sergius Paulus)bwanamkubwa wachiroma wa ku Kipro, anatembenuzidwandi Paulo...Mac 13:7-12

SESIBASARA (Sheshbazzar)kalonga wa Yuda...Ezara 1:8,11

SETI (Seth)mwana wachitatu wa Adamu...Gen 4:25ali mumndandanda wa makolo a Khristu...Luk 3:38

SIHORE (Shihor)dzina lopatsidwa kwa Nailo...Yes 23:3malire a Israeli chakumadzulo...Yos 13:3

SILISIYA (Cilicia)kwawo kwa Paulo...Mac 21:39ophunzira akumeneku anatsutsana ndi Stefano...Mac 6:9Paulo anagwirako ntchito...Agal 1:21

SILO (Shiloh)malo opembedzera...Ower 18:31Likulu la Kugawa ku dziko la malonjezano...Yos 18:1,10a Benjamini anamusowetsa mzimayi wakumeneku...Ower21:19-21Likasa la chipangano linatengedwa kuchokera kumeneku...1sam 4:3-11chilango chinaperekedwa...Yer 7:12-15— dzina la Mesiya...Gen 49:10

SINAI (Sinai)pa phiri (chimodzimodzinso ndi Horebu) pomwe Chilamulochinaperekedwa...Eks 19:1-25linagwiritsidwa ntchito mwa fanizo ndi Paulo...Agal 4:24,25

SING’ANGA (physician)kumeneko kulibe sing’anga...Yer 8:22alibwino sasowa sing’anga...Mat 9:12Luka, sing’anga wathu...Akol 4:14

SINJIRIRA (backbiting)osinjirira...Aro 1:30lilime losinjirira likwiyitsa nkhope...Miy 25:23

SINTHA (change)musintha nkhope yake...Yob 14:20iyeyu ndiwosasintha...Yob 23:13chifukwa safuna kusintha...Mas 55:19inu mumazisintha ngati chovala...Mas 102:26munthu wakuda nkusintha...Yer 13:23idzayesetsa kusintha masiku...Dan 7:25ndine Chauta wosasinthika...Malak 3:6ndikadasintha mau anga...Agal 4:20pakakhala kusintha paunsembe...Aheb 7:12umene udasinthapo milungu yake...Yer 2:11

SINTHA (exchange)adzaperekanji chosintha ndi moyo...Mat 16:26

SINTHANA (exchanged)siisinthanika ndi...Yob 28:17[onaninso: sandutsa]

SINTHIKA (transfigured)maonekedwe a Yesu anasinthika...Mat 17:2

SIRIONI (Sion)onani Ziyonidzina lopatsidwa ku mbali ya phiri la Heremoni...Deut 4:48

SIRIRA (covet)usasirire nyumba yake...Eks 20:17sindinasirira...Mac 20:33kapena ambala, kapena osirira...1 Akor 6:10okhala nao mtima ozolowera kusirira...2 Pet 2:14sizisamalira kanthu koma kusirira...Yer 22:17sichikadati chilamulo, usasirire...Aro 7:7

SIRIRA (covetousness)sizisamalira kanthu koma kusirira...Yer 22:17sichikadati chilamulo usasirire...Aro 7:7[onaninso: chisiriro, msiriro, kangamira]

Page 143: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

SIRIYA (Syria)fuko lachilendo kwa Israeli..2 Sam 8:11-13;10:8-19;1 Maf20:1-34;22:1-38;2 Maf 6:8-7:7anagonjetsedwa ndi Asiriya...2 Maf 16:9chionongeko chake chinanenedweratu...Yes 17:1-3uthenga wabwino unalalikidwa kwa iwo...Mac 15:23,41

SIRO-FENISIYA (Syro-Phoenicia)mwanawake wamkazi; anatulutsidwa ziwanda...Marko 7:25

SISERA (Sisera)mkulu wankhondo wachikenani wa gulu la nkhondo la Yabinianaphedwa ndi Yaele...Ower 4:2-22

SIYA (forsake)mukamsiya nayenso adzakusiyani...2 Mbir 15:2ngati ana ake asiya lamulo...Mas 89:30sadzawasiya okha osankhika...Mas 94:14ndikusasiya chilango cha...Miy 1:8amene sasiya zonse zimene ali...Luk 14:33[onaninso: leka]

SIYA (cease)kusachera kusiya...Miy 19:27[onaninso: leka]

SIYA (forsaken)Mulungu wanga mwandisiyiranji...Mas 22:1munthu wabwino atasiyidwa...Mas 37:25idzasiyidwa monga mizinda...Yes 17:9ndidaakusiya pakamphindi...Yes 54:7sudzatchedwanso ‘wosiyidwa’...Yes 62:4andisiya ine kasupe wa madzi...Yer 2:13Mulungu wanga mwandisiyiranji...Mat 27:46paja Dema adandisiya...2 Tim 4:10adasiya njira yolungama...2 Pet 2:15

SIYA (forsook)adasiya Mulungu mlengi wao...Deut 32:15adathawa, kumusiya yekha...Mat 26:56onse adangondisiya ndekha...2 Tim 4:16ndi chikhulupiriro anasiya Aigupto...Aheb 11:27

SIYA (leaves)amasiya nkhosa nayamba kuthawa...Yoh 10:12[onaninso: masamba]

SIYANA (differs)nyenyezizo zimasiyananso...1 Akor 15:41

SMIRINA (Smyrna)amodzi a malo a mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 1:11

SODOMU (Sodom)Loti anasankha kukhala kumeneku...Gen 13:10-13analandidwa ndi Kedorilaomere...Gen 14:8-24Abrahamu anampembedzera...Gen 18:16-33anaonongedwa ndi Mulungu...Gen 19:1-29ananenedwa kukhala chitsanzo cha uchimo ndichionongeko...Deut 29:23;32:32;Yes 1:9,10;3:9Yer 23:14; 49:18; Malir 4:6; Ezek 16:46-63;Mat 11:23,24; 2 Pet 2:6; Yud 7

SODZA (catch)nimuponye makoka anu kukasodza...Luk 5:4kuyambira tsopano udzakhala msodzi...Luk 5:10[onaninso: gwira, kola]

SOKERA (astray)anthu osokerera mtima...Mas 95:10ngakhale opusa sadzasokera...Yes 35:8

SOKONEZA (confuse)tisokoneze chinenedwe chao...Gen 11:7

SOKONEZA (confused)Yehova anasokoneza chinenedwe...Gen 11:9pakuti msonkhanowo unasokonezeka...Mac 19:32

SOKONEZA (confusion)nasokoneze iwo akundipangira...Mas 35:4

SOLOMONI (Solomon)mwana wa Davide kudzera mwa Bateseba...2 Sam 12:24anakhala mfumu...1 Maf 1:5-53analandira ndi kuchita malangizo a Davide...2 Maf 2anapempherera ndi kuwonetsera nzeru...1 Maf 3:3-28; 4:29-34anamanga ndi kupereka kwa Mulungu kachisi; anamanganyumba yachifumu...1 Maf 5-8Ambuye anaonekera kwa iye...1 Maf 9:1-9kutchuka kwake ndi ulemelero wake...1 Maf 9:10-10:29anagwa mu kupembedza mafano Mulungu adamchenjeza...1Maf 11:1-13adani ake...1 Maf 11:14-40imfa yake...1 Maf 11:41-43mabuku analembedwa mmalo mwake...Mas 72;127; Miy1:1;10:1; 25:1; Mlal 1:1; Nyim 1:1

SONKHANITSA (gather)sonkhanitsani pamaso panga anthu anga...Mas 50:5 adzasonkhanitsa tirigu wake...Mat 3:12ndikusonkhanitsa kumene sindinawaza...Mat 25:26nadzasonkhanitsa osankhidwa ake...Marko 13:27

SONKHANITSA (gathered)ndikusonkhanitsa pamodzi zamitundu...Mat 13:47adzasonkhanitsidwa pamaso pake...Mat 25:32

SONKHANITSA (gathers)adasonkhanitsa pamodzi madzi...Mas 33:7asonkhanitsa otayika a Israeli...Yes 56:8kusonkhanitsa pamodzi ana ako...Mat 23:37[onaninso: sonkhera]

SONKHERA (gathers)adzisonkhera zopanda pake...Mas 41:6[onaninso: sonkhanitsa]

SOPO (soap)ngakhale nsambire sopo...Yer 2:22

SOSA (prepared)mudasoseratu pookapo...Mas 80:9[onaninso: konzera]

SOSTENE (Sosthenes)wolamulira wa sunagoge ku Korinto...Mac 18:17— mbale wake wa Paulo mwa Ambuye...1 Akor 1:1

SOWA (destitute)pemphero la iwo akusowa...Mas 102:17akakhala wausiwa, m’chimsowa...Yak 2:15

SOWA (need)ndi kusowa zinthu zonse...Deut 28:48amadziwa zimene musowa...Mat 6:8Ambuye asowa iwo...Mat 21:3yense monga kusowa kwake...Mac 4:35wonditumikira pa chosowa...Afil 2:25adzakwaniritsa chosowa chanu...Afil 4:19kutithandiza nthawi ya kusowa...Aheb 4:16mbale wake ali wosowa...1 Yoh 3:17[onaninso: funa]

Page 144: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

SOWA (want)mbusa wanga, sindidzasowa...Mas 23:1

STEFANO (Stephen)mmodzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:1-8ananenedwa monama ndi Ayuda; anapereka mauodzitetezera...Mac 6:9-7:53anakhala Khristu woyamba kuzunzidwa...Mac 7:54-60

SUDZULA (divorce)alembe kalata ya chisudzulo...Deut 24:1kalata yake imene ndidasudzulira...Yes 50:1mkazi wake kalata ya chisudzulo...Marko 10:4

SUKOTI (Succoth)malo ena kummawa kwa Yordane...Ower 8:4,5malo okhala Yakobo...Gen 33:17— malo oyamba a zithando a Israeli...Eks 12:37

SULUFURE (sulphur) anagwetsa moto wa sulufure...Gen 19:24awazamo sulufure...Yob 18:15moto, utsi, ndi sulufure...Chiv 9:17yodzaza ndi miyala ya sulufure...Chiv 20:10

SUNGA (hold)umo unalandira nunamvamo nusunge nulape...Chiv 3:3[onaninso: gwira, gwidwa]

SUNGA (observe)sunga chifundo ndi chiweruzo...Hos 12:6kuwaphunzitsa asunge zinthu zonse...Mat 28:20musunga masiku ndi miyezi...Agal 4:10[onaninso: ona, penyetsetsa]

SUNGUNUKA (melt)a kumwamba adzasungunuka...Yes 34:4zidzayaka moto nkusungunuka...2 Pet 3:10zammwamba zidzasungunuka...2 Pet 3:12

SUNSA (dip)kusunsa nthongo yako...Rut 2:14ine ndidzamsunsira nthongo...Yoh 13:26

SUNSA (dipped)m’mene anasunsa nthongo adaitenga...Yoh 13:26[onaninso: viika]

SUZANA (Susanna)mzimai wokhulupirira yemwe anamtumikira Khristu...Luk

8:2,3

SWEKA (broken)monga chotengera chosweka...Mas 31:12koma moyo umasweka...Miy 15:13koma mzimu wosweka...Miy 17:22mtima wanga usweka...Yer 23:9[onaninso: phwanya]

SYASYALIKA (flatter)lilime lawo asyasyalika nalo...Mas 5:9[onaninso: kulankhula mochenjera]

T

TABERA (Taberah)chithando cha Israeli; ambiri anaphedwa ndi moto

pamenepo...Num 11:1-3

TABITA (Tabitha)wophunzira wa ku Yopa, wotchedwanso Dorika;anaukitsidwa...Mac 9:36-42

TABORI (Tabor)malo omwe anasonkhanira pamene ankamenyana ndiSisera...Ower 4:6,12,14

TADEYO (Thaddaeus)m’modzi wa khumi ndi awiri...Marko 3:18

TAKASA (churning)potakasa mkaka...Miy 30:33

TAKASUKA (broad)nandiika motakasuka...Mas 118:5[onaninso: takataka]

TAKATAKA (broad)iri yotakataka...Mat 7:13[onaninso: takasuka]

TAMANDA (praise)abale ako adzakutamanda...Gen 49:8mtamandeni pakuti ndi Mulungu...Deut 10:21ndidzakutamandani pa misonkhano...Mas 22:25ochita zolungama azitamanda...Mas 33:1pakamwa panga padzatamanda...Mas 34:1idzakutamandani mpaka muyaya...Mas 45:17azikutamandani ku Ziyoni...Mas 65:1mumtamande mwaulemu...Mas 66:2ya anthu idzakutamandani...Mas 67:3zoyenda m’menemo zitamande...Mas 69:34ndimatamanda inu nthawi zonse...Mas 71:6zakumwamba zimatamanda...Mas 89:5Mulungu amene ndimakutamandani...Mas 109:1ndimakutamandani kasanunkawiri...Mas 119:164oyera mtima adzakutamandani...Mas 145:10zamoyo zonse zitamanda...Mas 145:21tamandani Chauta...Mas 148:1chopuma chitamande Chauta...Mas 150:6wosadziwana naye akakutamandani...Miy 27:2ndipo udzanditamanda...Yes 60:18dziko lapansi lidzamtamanda...Yes 62:7pansi pano adzanditamanda...Yer 33:9makanda omwe kukutamandani...Mat 21:16alemekeze ndi kutamanda Mulungu...Afil 1:11ndidzakutamandani pamsonkhano...Aheb 2:12tamandani Mulungu wathu...Chiv 19:5

TAMANDA (praised)amene ayenera kumtamanda...2 Sam 22:4dzina la Chauta litamande...Mas 113:3woyenera kumtamanda...Mas 145:3makolo athu ankakutamandani...Yes 64:11apo ndidatamanda Mulungu...Dan 4:34Aisraeli amakutamandani...Mas 22:3tamandani Chauta...Mas 147:1nayenso amamtamanda...Miy 31:28ndipo adzatamanda Chauta...Yes 60:6kwambiri ndi zotamandika...Afil 4:8namaimba nyimbo zotamanda...Mas 84:4ankatamanda Mulungu...Luk 2:13nthawi ndi nthawi akutamanda...Luk 24:53

TAMARA (Tamar)mkazi wa Ere, mai ake a Perezi ndi Zera...Gen 38:6-30— mlongo wake wa Abisalomu...2 Sam 13:1-32

TAMBALA (rooster)tambala asanalire...Mat 26:75

TAMBASUKA (outstretched)ndi mkono wake wotambasula...Deut 23:21[onaninso: tambasula]

Page 145: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

TAMBASULA (outstretched)ndi mkono wake wotambasula...Deut 23:21[onaninso: tambasuka]

TANTHAUZIRA (explain)sanakhoza kutanthauzira mwambiwo...Ower 14:14[onaninso: fotokoza]

TANTHAUZIRA (explained)ankawatanthauzira zonse...Marko 4:34

TANTHAUZIRA (expounded)Yesu anayamba kuwatanthauzira...Luk 24:27

TANTHAUZIRA (interpret)kodi onse angathe kuzitanthauzira...1 Akor 12:30mphatsa ya kuchitanthauzira...1 Akor 14:13ndipo pakhale wina wotanthauzira...1 Akor 14:27ndipo wina afuna kutanthauzira...1 Akor 14:26

TANTHAUZO (interpretation)tanthauzo lake la maloto...Gen 40:12wina mphatso ya kutanthauzira...1 Akor 12:10chitanthauzidwa pachokha...2 Pet 1:20[onaninso: chimasuliro]

TAPENESI (Tahpanhes)mzinda wa Ejipito, malo othawirako Ayuda...Yer2:16;44:1;Ezek 30:18

TARISISI (Tarshish)mzinda umene unali patali ndi Palistina...Yon 1:3zombo zake zinaonongedwa...Mas 48:7

TARISO (Tarsus)kumene Paulo anabadwira...Mac 21:39Paulo anatumizidwako...Mac 9:30Banabasi anapitako...Mac 11:25

TATENAI (Tattenai)bwanankubwa wa ku Perisiya yemwe ankatsutsana ndiAyuda...Ezara 5:3,6

TAYA (cast)titaye nsinga zao...Mas 2:3koma mwatitaya...Masalimo 44:9musanditaye kundichotsa pamaso panu...Mas 51:11tayani ndi kudzichotsera...Ezek 18:31mudzataya zochimwa zawo...Mika 7:19anawo a ufumu adzatayidwa...Mat 8:12wakudza kwa ine sindidzamtaya...Yoh 6:37Mulungu anataya anthu ake kodi...Arom 11:1potero musataye kulimbika...Aheb 10:35[onaninso: gwetsa]

TAYA (casting)ndikutaya pa iye nkhawa...1 Pet 5:7chikondi changwiro chitaya...1 Yoh 4:18[onaninso: kugwetsa]

TAYA (gives)mbusa wabwino ataya moyo wake...Yoh 10:11[onaninso: patsa]

TAYA (lose)yakusunga ndi mphindi yakutaya...Mlal 3:6kupulumutsa moyo wake adzautaya...Mat 16:25kuti mungataye zimene tazichita...2 Yoh 8dziko lonse, nataya moyo wake...Mat 16:26ngati itayika imodzi...Luk 15:8kusunga moyo wake adzautaya...Luk 17:33zonse zikhale chitayiko... Afil 3:8

TAYA (rejected)Israeli wachitaya chokoma...Hos 8:3[onaninso: kana, kanidwa, kanizidwa]

TAYA (rejects)chifukwa chake iye wakutaya ichi...1 Ates 4:8[onaninso: kana]

TAYIKA (lost)chiyembekezo chathu chitayika...Ezek 37:11kudzapulumutsa amene adatayika...Mat 18:11pakutayika imodzi ya 100...Luk 15:4nkhosa yanga yotayikayo...Luk 15:6ndinapeza ndalama ndidatayayo...Luk 15:9sanatayika m’modzi yense wa iwo...Yoh 17:12sindinataya m’modzi...Yoh 18:9

TAYA MTIMA (discouraged)sadzafookera kapena kutaya mtima...Yes 42:4ana anu, kuti angataye mtima...Akol 3:21musafookere ndi kutaya mtima...Aheb 12:3

TAYIKA (adrift)wotayika pakati...Mas 88:5

TAYIKA (perish)tatayika tonsefe taferatu...Num 17:12zotsimikiza mtima zake zitayika...Mas 146:4adzatikumbukira tingatayike...Yon 1:6m’modzi wa ang’ono awa atayike...Mat 18:14wokhulupirira mwa Iye asatayike...Yoh 3:16[onaninso: onongedwa, onongeka]

TAYIKITSA (suffered)ndinatayikitsa zinthu zonse...Afil 3:8[onaninso: kumva zowawa]

TCHEDWA (called)ndakutchula dzina lako...Yes 43:1adzatchedwa M’nazarayo...Mat 2:23kuti titchedwe ana a Mulungu...1Yoh 3:1[onaninso: itana, itanidwa, itcha]

TCHIKA (bed)tanyamuka nutenge tchika lako...Mat 9:6[onaninso: kama, mphasa, pogona]

TCHIMO (sin)Iye adafera tchimo...Num 32:23sadachitepo tchimo...1 Pet 2:22kuti tilibe tchimo...1 Yoh 1:8wake akuchita tchimo...1 Yoh 5:16chosalungama ndi tchimo...1 Yoh 5:17[onaninso: chimwa, uchimo]

TCHINGA (hedge)taonani, ndidzatchinga njira...Hos 2:6wolasa ngati tchinga laminga...Mika 7:4[onaninso: mpanda]

TCHINJIRIZA (guard)kutchinjiriza mtengo wopatsa moyo...Gen 3:24[onaninso: teteza]

TCHULA (remember)koma ife tidzatchula dzina...Mas 20:7tidzatchula chikondi chako...Nyi 1:4[onaninso: kumbukira]

TEKOWA (Tekoa)kwawo kwa mkazi wanzeru...2 Sam 14:2,4,9

Page 146: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kwawo kwa Amosi...Amo 1:1

TEMANI (Teman)fuko, kummawa kwa Edomu...Gen 36:34chiweruzo chinanenedwa pa iye...Amo 1:12Mulungu anaonekera kuchokera pamenepa...Hab 3:3

TEMBENUKA (converted)ngati simutembenuka...Mat 18:3

TEMBERERA (curse)sindidzatembereranso konse nthaka...Gen 8:21kutemberera mkulu wa anthu...Eks 22:28usamatemberera wogontha...Lev 19:14nunditembererere anthu awa...Num 22:6usawatemberera konse...Num 23:25koma atemberera mumtima...Mas 62:4atemberera za m’nyumba ya woipa...Miy 3:33usatemberere mfumu...Mlal 10:20usatemberere wolemera...Mlal 10:20[onaninso: temberero]

TEMBERERA (curses)ndikutemberera akutemberera iwe...Gen 12:3aliyense wakutemberera...Lev 20:9wotemberera atate ake...Miy 20:20

TEMBEREREDWA (accursed)wopachikidwa pamtengo atembereredwa...Deut 21:23zaka zana limodzi atembereredwa...Yes 65:20likhala lotembereredwa...Yoh 7:49ndekha nditembereredwa...Aro 9:3onena Yesu ngwotembereredwa...1 Akor 12:3akhale wotembereredwa...Agal 1:8

TEMBEREREDWA (cursed)wotembereredwa ndiwe...Gen 3:14wotembereredwa munthu amene...Yer 17:5atembereredwa iye amene agwira...Yer 48:10chokani kwa ine otembereredwa...Mat 25:41nitsala pang’ono ikadatembereredwa...Aheb 6:8

TEMBERERO (curse)anakusandulizirani temberero likhale...Deut 23:5ndidzakutumizirani temberero...Malaki 3:9za lamulo liwakhalira temberero...Agal 3:10[onaninso: temberera]

TENGA (carried)natengedwa kunka kumwamba...Luk 24:51ndipo ananditenga...Chiv 17:3[onaninso: nyamula]

TENGA (carry)muwatenga ngati ndi madzi...Mas 90:5[onaninso: nyamula, senza]

TENTHA (burn)ndi kutentha agareta awo...Yos 11:6sanali wotentha mkati mwathu...Luk 24:32ntchito ya wina itenthedwa...1 Akor 3:15thupi langa alitenthe...1 Akor 13:3ndicho kutenthedwa...Aheb 6:8amatenthedwa...Aheb 13:11ziri momwemo zizatenthedwa...2 Pet 3:10[onaninso: ipsa]

TENTHA (burning)ndi kutentha thupi...Deut 28:22ngati moto wotentha...Yer 20:9[onaninso: psereza]

TENTHA (consumed)moto wa Yehova unagwa nutentha...1 Maf 18:38[onaninso: itha, nyeka, ononga]

TENTHA (hot)sindinunso otentha...Chiv 3:16

TENTHA (strike)kapena silidzawatentha dzuwa...Chiv 7:16[onaninso: kantha, menya, panda, wamba]

TEOFILO (Theophilus)Luka amalembera mabuku ake kwa iye...Luk 1:3; Mac 1:1

TERA (Terah)atate a Abrahamu...Gen 11:26wopembedza mafano...Yos 24:2anafera ku Harani...Gen 11:25-32

TERTULO (Tertullus)wolankhulira anthu pa milandu yemwe anamuimba mlanduPaulo...Mac 24:1-8

TESALONIKA (THESSALONICA)Paulo analalikirako...Mac 17:1-13Paulo analemba kalata ku mipingo ya kumeneko...1 Ates 1:1

TETEZA (defend)Mulungu wa Yakobo akuteteze...Mas 20:1tetezeni kwa anthu ondiukira...Mas 59:1Inu tetezani anthu ofooka ndi amasiye...Mas 82:3tetezani ana amasiye, muwaimirire...Yes 1:17ndipo sateteza aumphawi...Yer 5:28[onaninso: chinjiriza, umirira]

TETEZA (guard)wa Israeli adzidzakutetezani...Yes 52:12[onaninso: tchinjiriza]

THAMANGA (run)ndidzathamangira njira ya malamulo...Mas 119:32adzathamanga koma osatopa...Yes 40:31adzathamangira uku ndi uko...Dan 12:4ndimathamanga monga munthu...1 Akor 9:26kuti kapena ndithamange...Agal 2:2sindidathamange pachabe...Afil 2:16tithamange ndi khama...Aheb 12:1mwaleka kuthamanga nao...1 Pet 4:4

THAMBO (heavens)ndi kusandutsa thambo lanu likhale...Lev 26:19ndi kulenga thambo la m’mwamba latsopano...Yes 65:17kuthambo kunatseguka...Mat 3:16[onaninso: kumwamba, miyamba, mlengalenga]

THANDIZA (help)tithandizeni kumsautsa...Mas 60:11fulumilani kundithandiza...Mas 71:12thandizani kusakhulupirira...Marko 9:24mumuuze tsono kuti andithandize... Luka 10:40chisomo chakutithandiza nthawi...Aheb 4:16[onaninso: mthandizi, thandizo]

THANDIZA (helped)kufikira pano Yehova anatithandiza...1 Sam 7:12koma Yehova anandithandiza...Mas 118:13tsiku la chipulumutso ndakuthandiza...Yes 49:8wathandiza anthu ake...Luk 1:54mumthandize m’zinthu zirizonse...Arom 16:2Mzimu athandiza zofooka zathu...Arom 8:26mphamvu za machiritso, mathandizo...1 Akor 12:28

Page 147: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

THANDIZO (help)ndiye chikopa cha thandizo lako...Deut 33:29mulibe thandizo mwa ine ndekha...Yob 6:13thandizo lotuluka m’malo oyera...Mas 20:2iye ndiye thandizo lathu...Mas 33:20thandizo lopezekeratu m’masatso...Mas 46:1ndasenza thandizo pa chiphona...Mas 89:19akadapanda kukhala thandizo...Mas 94:17thandizo langa lidzera kuti...Mas 121:1thandizo langa lidzera kwa Yehova...Mas 121:2thandizo lathu liri m’dzina la Yehova...Mas 124:8[onaninso: mthandizi, thandiza]

THANTHAWE (rock)pafupi ndi thanthwe...Eks 17:6namenya thanthwe kawiri...Num 20:11mwaleka Thanthwe limene linakubalani...Deut 32:18popeza thanthwe lao nlosanga...Deut 32:31palibe thanthwe lina...1 Sam 2:2Yehova ndiye thanthwe langa...2 Sam 22:2palibe thanthwe lina...2 Sam 22:32litamandike thanthwe langa...2 Sam 22:47thanthwe limasendezeka...Yob 14:18adzanditeteza pa thanthwe...Mas 27:5ndinu thanthwe langa...Mas 31:3munditsogolere ku thanthwe...Mas 61:2Mulungu ndiye thanthwe...Mas 94:22Iye anasandutsa thanthwe...Mas 114:8iye amene ndiye thanthwe...Yes 17:10ngati mthunzi wa thanthwe...Yes 32:2nyumba yake pa thanthwe...Mat 7:24ndipo pa thanthwe limeneli...Mat 16:18pa nthaka ya pa thanthwe...Luk 8:6thanthwe limene lidzawagwetsa...Arom 9:33anali kumwa m’thanthwe...1 Akor 10:4

THAWA (escape)thawirani kumapiri...Gen 19:17ndi pothawira padzawasowa...Yob 11:20[onaninso: pulumuka, pulumutsidwa]

THAWA (fled)nyanja idaona zimenezi nithawa...Mas 114:3amene tidathawira kwa iye...Aheb 6:18

THAWA (flee)wathawiranji iwe mobisika...Gen 31:27akuda inu athawe...Num 10:35munthu ngati iwe nkuthawa kodi...Neh 6:11akundipenya pabwalo anandithawa...Mas 31:11kapena ndidzathawira kuti...Mas 139:7M’yudeya athawire kumapiri...Mat 4:16thawani dama, tchimo lililonse...1 Akor 6:18munthu wa Mulungu, thawa izi...1 Tim 6:11mdierekezi, ndipo adzakuthawani...Yak 4:7

THEBESI (Thebes)Mzinda wa Nineve...Nah 3:8

THEKA (possible)nzotheka ndi Mulungu...Mat 19:26zimatheka ndi Mulungu...Luk 18:27sangathe kuchotsa machimo...Aheb 10:4

THEMBERERO (oath)anthuo ankaopa themberero...1 Sam 14:26ndi chitemberero ndi chitonzo...Yer 42:18[onaninso: lumbira, lumbiro]

THETSA (abolished)zimene mudapanga zidatheratu...Ezek 6:6Iye adathetsa malamulo...Aef 2:15

Khristu adathetsa mphamvu...2 Tim 1:10

THETSA (canceal)amafuna kuthetseratu kunyada...Yob 33:17

THIRA (pour)thirirani mkwiyo wanu...Mas 79:6ndidzathira madzi pa...Yes 44:3[onaninso: tsanulira]

THIRA (poured)iwo anathira pemphero...Yes 26:16Iye anathira moyo wake ku imfa...Yes 53:12[onaninso: thiridwa, tsanulidwa, tsanulira]

THIRIDWA (poured)ndathiridwa pansi monga...Mas 22:14ukali wanga udzathiridwa pamalo...Yer 7:20ngatinso ndithiridwa pa nsembe...Afil 2:17pakuti ndirinkuthiridwa nsembe...2 Tim 4:6[onaninso: thira, tsanulidwa, tsanulira]

THODWA (weary)nadzithodwetsa kuchita zoipa...Yer 9:5[onaninso: lema, topa,]

THOKOZA (thank)ndikukuthokozani ndi kukutamandani...Dan 2:23ungamthokoze wantchitoyo...Luk 17:9ndikuthokoza Mulungu...Aro 1:8nathokoza Mulungu...Mat 26:27

THOKOZA (thanksgiving)molimbika nyimbo yothokoza...Mas 26:7nsembe zanu zothokozera...Mas 50:14pamaso pake, tikamthokoze...Mas 95:2zipata zake mukuthokoza...Mas 100:4[onaninso: chiyamiko]

THUMBA (bag)chaikidwa mthumba...Yob 14:17kulipirako mthumba lobooka...Hag1 :6kapena thumba lakamba...Mat 10:10

THUNTHU (complete)mudapatsidwa moyo wonse wathunthu...Akol 2:10[onaninso: tsiriza]

THUPI LA PADZIKO (celestial)ndi ulemerero wa lapadziko...1 Akor 15:40

THUPI (bodily)maonekedwe a thupi lake ngati nkhunda...Luk 3:22maonekedwe a thupi lake...2 Akor 10:10chidzalo cha umulungu m’thupi...Akol 2:9chizolowezi cha thupi...1Tim 4:8

THUPI (body)thupi lathu langoti thapsa...Mas 44:25thupi lake likunga...Nyi 5:14thupi lake limakhathamira...Dan 4:33diso ndilo nyali ya thupi...Mat 6:22musamaopa amene akupha thupi...Mat 10:28ichi ndi thupi langa...Mat 26:26atafundira pathupi...Marko 14:51iye anali kunena kachisi wa thupi...Yoh 2:21adzandilanditsa ndani mthupi la imfa...Aro 7:24ndiwo chiomboledwe cha thupi lathu...Aro 8: 23pakuti monga m’thupi limodzi...Aro 12:4Ambuye wa thupi...1 Akor 6:13achimwira thupi lake...1 Akor 6:18simudziwa kuti thupi lanu lili...1 Akor 6:19

Page 148: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

lemekezani Mulungu m’thupi lanu...1 Akor 6:20ndipumphuntha thupi langa...1 Akor 9:27ndife thupi limodzi...1 Akor 10:17ili ndi thupi langa...1 Akor 11:24mlandu wonyoza thupi la Ambuye...1 Akor 11:27pakuti monga thupi lili limodzi...1 Akor 12:12pakutinso thupi silikhala chiwalo...1 Akor 12:14koma inu ndinu thupi la Khristu...1 Akor 12:27angakhale ndipereka thupi langa...1 Akor 13:3lifesedwa thupi lachibadwidwe...1 Akor 15:44mthupi limodzi mwa mtandawo...Aef 2:16Khristu adzakuzidwa mthupi...Afil 1:20mthupi lake la imfalo...Akol 2:11ndi kusalabadira thupi...Akol 2:23munaitanidwa mthupi limodzi...Akol 3:15koma thupi mundikonzera ine...Aheb 10:5mwachopereka cha thupi la...Aheb 10:10monga thupi lopanda mzimu...Yak 2:23machimo athu mwini yekha m’thupi...1 Pet 2:24[onaninso: mtembo]

THUPI (flesh)awiriwo amakhala thupi limodzi...Gen 2:24m’thupi langa lomweli ndidzamuona...Yob 19:26thupi langanso lidzakhala pabwino...Mas 16:9mtima wanga ndi thupi langa...Mas 84:2kuphunzira kwambiri kutopetsa thupi...Mlal 12:12pakuti thupi ndi mwazi...Mat 16:17ndipo awiriwo adzakhala thupi limodzi...Marko 10:8mau asandulika thupi...Yoh 1:14ndiwo thupi langa...Yoh 6:51ngati simukudya thupi langa...Yoh 6:63inu muweruza monga mwa thupi...Yoh 8:15pakuti pamene tinali m’thupi...Aro 7:5ndi thupi nditumikira lamulo...Aro 7:25iwo amene ali monga mwa thupi...Aro 8:5koma inu simuli m’thupi ai...Aro 8:9ndi moyo monga mwa thupi...Aro 8:13thupi lili lonse losadzitamanda...1 Akor 1:29adzakhala thupi limodzi...1 Akor 6:16thupi lilakalaka potsutsana...Agal 5:17adapachika thupi ndi zotsutsa...Agal 5:24kuonekera okoma m’thupi...Agal 6:12kuti akadzitamandire m’thupi...Agal 6:13Khristu adamva zowawa mthupi...1 Pet 4:1simukhalanso ndi moyo m’thupi...1 Pet 4:2chilakolako cha thupi...1 Yoh 2:16kuti Yesu Khristu anadza m’thupi...1 Yoh 4:2[onaninso: anthu, mnofu]

THUPI (fleshly)si nzeru ya thupi...2 Akor 1:12la lamuliro la kwa thupi...Aheb 7:16mudzikanize zilakolako za thupi...1 Pet 2:11

THYASIKA (flatters)amene amathyasika mnzanga...Miy 29:5

THYOLA (pluck)mubudule ngala ndi dzanja lanu...Deut 23:25azithyola nawo zipatso...Mas 80:12ngati sakumva ndidzazula mtundu...Yer 12:17adayamba kuthyolako ngala...Mat 12:1anayamba kubudula ngala...Marko 2:23

THYOLA (plucked)ndipo ndinathyola nsagwada...Yob 29:17ankathyolako ngala...Luk 6:1[onaninso: kolowola, kudzula]

TIANA (babes)mphunzitsi wa tiana...Aro 2:20

TIATIRA (Thyatira)kumene amakhala Lidia...Mac 16:14amodzi a malo a mipingo isanu ndi iwiri...Chiv 2:18-24

TIBERIASI (Tiberias)nyanja ya Galileya...Yoh 6:1,23

TIGILATI-PILESERE (Tiglath-Pileser)mfumu yamphamvu ya Asiriya yomwe inagonjetsaSamariya...2 Maf 15:29

TIKIKO (Tychicus)mnzake wa Paulo...Mac 20:1,4wotumikira Paulo...Aef 6:21,22;Akol 4:7-9;2 Tim 4:12

TIMBEU TONUNKHIRA (mint)chachikhumi cha timbeu tonunkhira...Mat 23:23

TIMONI (Timon)mmodzi wa atumiki asanu ndi awiri...Mac 6:1-5

TIMOTEO (Timothy)mnzake woyenda naye wa Paulo...Mac 16:1-3;18:5; 20:4,5;2 Akor 1:19; Afil 1:1;2 Tim 4:9,21amatumikira payekha...Mac 17:14,15; 19:22;1 Akor 4:17;Afil 2:19,23; 1 Ates 3:1-6;1Tim 1:1-3; 4:14

TINDALAMA (mites)wamasiye akuponya tindalama...Luk 21:1

TIRIGU (grain)ng’ombe imene ikupuntha tirigu...Deut 25:4muwameretsera tirigu...Mas 65:9womana tirigu anthu amtemberera...Miy 11:26nadzatsitsimuka ngati tirigu...Hos 14:7tirigu adzakometsera anyamata...Zek 9:17pakati pa minda ya tirigu...Mat 12:1ngati mbeu ya tirigu siigwa...Yoh 12:24pamene ikupuntha tirigu...1 Akor 9:9

TIRIGU (wheat)wosalala wa tirigu...Mas 81:16tigulitsenso tirigu...Amo 8:5mungu womwe wa tirigu...Amo 8:6musonkhanitse tirigu...Mat 13:30mbeu ya tirigu...Yoh 12:24kaya ndi ya tirigu...1 Akor 15:37ufa wosalala ndi tirigu...Chiv 18:13

TITO (Titus)anatumikira ku Krete...Tit 1:4,5nthumwi ya Paulo ku Korinto...2 Akor 7:6,7,13,14; 8:6-23

TIZA (Tirzah)kumene Yeroboamu amalamulira...1 Maf 14:17likulu la Israeli kufikira nthawi ya ulamuliro wa Omuri...1Maf 16:6-23

TOBIYA (Tobia)wantchito wa m’amoni; anachita chipongwe Ayuda...Neh 2:10

TOFETI (Tophet)pakuti Tofeti wakonzedwa kale...Yes 30:33yotchedwa Tofeti...Yer 7:31ndidzausandutsa ngati Tofeti...Yer 19:12ngati za ku Tofeti...Yer 19:13

TOMASI (Thomas)mtumwi wa Khristu...Mat 10:3anakonzeka kukafa naye limodzi Khristu...Yoh 11:16anakaikira kuuka kwa Khristu...Yoh 20:24-29

Page 149: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

TONTHOZA (comfort)ndikuti, mudzanditonthoza liti...Mas 119:82mutonthoze, mutonthoze mtima wa...Yes 40:1Yehova watonthoza mtima...Yes 51:3ndikatonthoze mtima wa onse...Yes 61:2mulibe m’modzi wakuutonthoza...Malio 1:2chitonthozo chimene titonthozedwa nacho...2 Akor 1:4ngati tsono muli chitonthozo mwa Khristu...Afil 2:1[onaninso: sangalatsa]

TONTHOZA (comforted)Yehova watonthoza mtima wa anthu...Yes 49:13ulibe wakuutonthoza...Malio 1:9[onaninso: tonthozedwa]

TONTHOZA (comforts)ngati wotonthoza ofedwa...Yob 29:25ndine amene nditonthoza mtima wako...Yes 51:12olira maliro ake zotonthoza mtima...Yes 57:18munthu amene amake amamtonthoza...Yes 66:13tidzathe ife kutonthoza iwo...2 Akor 1:4iye amene atonthoza adzichepese...2 Akor 7:6

TONTHOZEDWA (comforted)Isake anatonthozedwa mtima...Gen 24:67mtima wanga unakana kutonthozedwa...Mas 77:2akana kutonthozedwa mtima...Yer 31:15[onaninso: tonthoza]

TONZEDWA (blasphemed)mukatonzedwa pa dzina la Mulungu...1 Pet 4:14[onaninso: mwano, nyoza]

TOPA (weary)ine ndatopa nawo...Gen 27:46kuwopa kuti angatope...Miy 25:17ozizira kwa munthu otopa...Miy 25:25mmodzi yemwe wodzatopa...Yes 5:27otopa apumule...Yes 28:12adzathamanga koma osatopa...Yes 40:31[onaninso: lema]

TROASI (Troas)pamene Paulo analandira masomphenya ake...Mac 16:8-11

TSALA (abide)ndipo tsopano zitsala chikhulupiriro, chiyembekezo...1 Akor13:13[onaninso: khala]

TSAMBA (leaf)munali tsamba lazitona...Gen 8:11mudzaopsa tsamba lakungouluka...Yob 13:25koma tsamba lake likhala...Yer 17:8

TSAMIRA (lean)chifukwa cha ndalama koma atsamira pa Yehova...Mik 3:11[onaninso: dalira]

TSANULIDWA (poured)mafuta onunkhira otsanulidwa...Nyim 1:3ukali wake utsanulidwa ngati moto...Nah 1:6chikondi cha Mulungu chinatsanulidwa...Aro 5:5[onaninso: thira, thiridwa, tsanulira]

TSANULIRA (pour)tsanurirani mitima yanu...Mas 62:8thambo litsanulire pansi chilungamo...Yes 45:8tsanulirani ukali wanu...Yer 10:25ndidzasanulira mzimu wanga pa...Yow 2:28ndipo ndidzasanulira pa nyumba...Zek 12:10

tsanulirani kudziko mbale...Chiv 16:1[onaninso: thira]

TSANULIRA (poured)udzitsanulira mkati mwanga...Yob 30:16anakutsanulirani chisomo pa milomo...Mas 45:2nawatsanulira pamutu pake...Marko 14:3amene anatsanulira pa ife...Tit 3:6[onaninso: thira, thiridwa, tsanulidwa]

TSATA (follow)chilungamo ndicho muzichitsata...Deut 16:20mverani Ine inu amene mutsata...Yes 51:1mphunzitsi, ndidzakutsatani...Mat 8:19nanena kwa iye, nditsate ine...Mat 9:9nanyamule mtanda wake nanditsate...Marko 8:34chifukwa sanali kutsata ife...Marko 9:38koma mlendo sidzidzamtsata...Yoh 10:5anditumikira Ine, anditsate...Yoh 12:26koma enanso ziwatsata...1 Tim 5:24ndiwo amene atsata...Chiv 14:4ntchito zao zitsatana nao...Chiv 14:13[onaninso: londola]

TSATA (follows)koma ine ndinamtsata Yehova...Yos 14:8Yehova ananditenga ndili kutsata...Amo 7:15ndipo tinakutsatani Inu...Marko 10:28wonditsata Ine sadzayenda...Yoh 8:12

TSAYA (cheek)apereke tsaya lake...Malio 3:30ngati munthu akumenya patsaya...Mat 5:39

TSAYA (cheekbone)mwapanda adani anga patsaya...Mas 3:7

TSEGULA (open)ndi kukutsegulira milomo...Yob 11:5tsegula pakamwa pako...Miy 31:8chiwanda chikhoza kumtsegulira...Yoh 10:21[onaninso: fumbatula, tsekuka, tsekula]

TSEKA (closed)wakutsekano maso...Yes 29:10pakuti mauwo atsekedwa...Dan 12:9

TSEKEREZA (confine)lembo linatsekereza...Agal 3:22

TSEKUKA (open)maso ao adatsekuka...Luk 24:31ndinaona kumwamba kutatsekuka...Chiv 19:11[onaninso: fumbatula, tsegula, tsekula]

TSEKULA (open)akadzatsekula palibe amene...Yes 22:22ndipo tatsekula mtima wathu...2 Akor 6:11[onaninso: fumbatula, tsegula, tsekuka]

TSEKULA (opens)anawatsekula makutu anthuwo...Yob 33:16anatsekula maso a anthu...Mas 146:8iyeyo mlonda amatsekulira...Yoh 10:3amene amati akatsekula...Chiv 3:7

TSIKA (descend)ulemu wake sutsika naye...Mas 49:17atsike tsopano pa mtanda...Marko 15:32Ambuye adzatsika kumwamba...1 Ates 4:16sindiyo yotsika kumwamba...Yak 3:15popeza Yehova anatsikira...Eks 19:18

Page 150: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

anatsikiranso kumadera...Aef 4:9iye wotsikayo ndiye yemweyo...Aef 4:10

TSIKA (descending)analimkutsika pamenepo...Gen 28:12ndinaona Mzimu ali kutsika...Yoh 1:32natsikira pa mwana wa munthu...Yoh 1:51wotsika m’mwamba kuchokera...Chiv 21:10

TSIKIMIZA (affirm)mau otsikimiza...Tit 3:8[onaninso: tsimikizika]

TSIKIRA (go)iwo akutsikira kunyanja...Mas 107:23[onaninso: pita]

TSIKU NDI TSIKU (daily)nadzadikira pazitseko zanga tsiku ndi tsiku...Miy 8:34iwo andifuna ine tsiku ndi tsiku...Yes 58:2tsiku ndi tsiku ndimakhala m’kachisi...Mat 26:55nanyamule mtanda wake tsiku ndi tsiku...Luk 9:23ndifa tsiku ndi tsiku...1 Akor 15:31aliyense amaima tsiku ndi tsiku...Aheb 10:11[onaninso: masiku onse]

TSIKU LOBADWA (birthday)ndilo tsiku lakubadwa kwake kwa Farao...Gen 40:20tsiku lakubadwa kwake kwa Herode...Marko 6:21

TSIKU (day)mudzisunga tsiku lino...Eks 12:17uzikumbukira tsiku la sabata...Eks 20:8natemberera tsiku lake...Yob 3:1tsiku limodzi m’mabwalo anu...Mas 84:10tsiku ili ndilo adaliika Yehova...Mas 118:24popeza sudziwa tsiku lina...Miy 27:1tsiku la Yehova ndilalikuru...Yow 2:11inu akutalikitsa tsiku loipa...Amo 6:3tsiku la Yehova layandikira...Zef 1:7tsiku la tinthu tating’ono...Zek 4:10ndani adzapirira tsiku lakudza...Malaki 3:2tsiku lakuweruza mlandu...Mat 10:15lisanadze tsiku la Ambuye...Mac 2:20kuti tsiku lina liposa linzake...Aro 14:5pakuti tsikulo lidzaisonyeza...1 Akor 3:13anaukitsidwa tsiku lachitatu...1 Akor 15:4tsiku la Ambuye lidzaza monga...1 Ates 5:2tsiku limodzi likhala kwa Ambuye...2 Pet 3:8[onaninso: usana]

TSIMIKIZA (confirm)adatisimikiza kukhulupirikako...Aro 15:8adatitsimikizira kuti ndi oona...Aheb 2:3Mulungu pofuna kuwatsimikizira...Aheb 6:17ndipo ankatsimikiza mau ao...Marko 16:20[onaninso: limbitsa]

TSIMIKIZIDWA (attested)Mulungu adakutsimikizirani zimenezi...Mac 2:22

TSIMIKIZIDWA (stand)adzadziwa ngati adzatsimikizidwa mau a yani...Yer 44:28[onaninso: chirimika, ima, khala, khazikika, limba, uka]

TSIMIKIZIKA (affirm)mau otsimikizika...Tit 3:8[onaninso: tsikimiza]

TSINDE (stem)idzaphuka pa tsinde...Yes 11:1

TSIRIZA (complete)ntchito yabwino, adzaitsiriza...Afil 1:6watsirizika mkwiyo wa Mulungu...Chiv 15:1[onaninso: thunthu]

TSIRIZA (end)potsiriza adzakhala oipa...2 Pet 2:20kuchita mpaka potsiriza...Chiv 2:26woyamba ndi wotsiriza...Chiv 22:13[onaninso: chimaliziro,chitsiriziro, itha, maliza, mathero,matsiriziro]

TSIRIZA (finish)anandipatsa ndizitsirize...Yoh 5:36kotero kuti ndikatsirize njira yanga...Mac 20:24m’mene ndinatsiriza ntchito...Yoh 17:4ndatsiriza bwino mpikisano...2 Tim 4:7[onaninso: maliza]

TSITSA (humiliation)wolemera nayenso anyadire pamene Mulungu amtsitsa...Yak

1:10[onaninso: chititsa manyazi, peputsa]

TSITSI (hair)tsitsi la thupi langa lidati nyau...Yob 4:15tsitsi lako likunga gulu la mbuzi...Nyi 4:1kapena kulidetsa bii tsitsi...Mat 5:36silidzaonongeka tsitsi limodzi...Luk 21:18ngati mkazi asunga tsitsi...1 Akor 11:15osati ndi tsitsi lake loluka...1 Tim 2:9tsitsi longa tsitsi la akazi...Chiv 9:8

TSITSI (hairs)ziposa tsitsi la mutu wanga...Mas 40:12ndipo ngakhale mpaka tsitsi la imvi...Yes 46:4tsitsi lonse la m’mutu mwanu...Mat 10:30[onaninso: imvi]

TSITSIMUTSA (revival)kutitsitsimutsa kwa kanthawi...Ezara 9:8

TSITSIMUTSA (revive)mudzanditsitsimutsanso inu amene...Mas 71:20ndi kutsitsimutsa mtima wa osweka...Yes 57:15posachedwa adzatitsitsimutsa...Hos 6:2Yehova tsitsimutsani ntchito yanu...Hab 3:2[onaninso: patsanso moyo]

TSOGOLERA (guide)adzakhala wotitsogolera...Mas 48:14wotsogolera ubwana wanga...Yer 3:4kudzatitsogolera pa njira ya...Luk 1:19adzatsogolera inu mchoonadi...Yoh 16:13wokhala mtsogoleri wa iwo omwe...Mac 1:16uli wotsogolera wa akhungu...Aro 2:19

TSOGOLERA (lead)munditsogolera mchoonadi...Mas 25:5ndipo nditsogolereni...Mas 31:3dzanja lanu lidzanditsogolera...Mas 139:10wakhungu mkutsolera wakhungu...Luk 6:39anditsogolera ku madzi odikha...Mas 23:2anditsogolera m’mabande a chilungamo...Mas 23:3ngati wa khungu amtsogolera...Mat 15:14iye yekha maina ao, nazitsogolera...Yoh 10:3[onaninso: mtovu]

TSOGOLERA (led)Yehova yekha anatsogolera...Deut. 32:12anawatsogolera panjira yolunjika...Mas 107:7[onaninso: tsogozedwa]

Page 151: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

TSOGOZEDWA (led)onse amene atsogozedwa ndi Mzimu...Aro 8:14[onaninso: tsogolera]

TSOKA (adversity)tsiku la tsoka lingilira...Mlal 7:14[onaninso: masautso]

TSOKA (calamity)inetu ndidzachitira chiphwete tsoka lanu...Miy 1:26chifukwa chake tsoka lake lidzadza modzidzimutsa...Miy 6:15[onaninso: chiwonongeko, choipa]

TSOKA (disaster) tsoka lidzatsatana ndi... Ezek 7:26[onaninso: choipa, kuonongeka, tsoka]

TSOPANO (again)kubadwa mwatsopano...Yoh 3:7amkana Mulungu tsopano...Aheb 6:6

TSOPANO (new)inalowa mfumu yatsopano...Eks 1:8akalenga chinthu chatsopano...Num 16:30anasankha milungu yatsopano...Ower 5:8palibe katsopano pano...Mlal 1 :9ndidzachita chinthu chatsopano...Yes 43:19ndilenga kumwamba kwatsopano...Yes 65:17chioneke chatsopano m’mawa...Mali 3:23sathira vinyo watsopano...Mat 9:17inu lamulo latsopano...Yoh 13:34kapena kumva chatsopano...Mac 17:21ali wolengedwa watsopano...2 Akor 5:17ndipo munavala pangano latsopano...Akol 3:10ndidzapangana pangano latsopano...Aheb 8:8miyamba yatsopano...2 Pet 3:13dzina latsopano lolembedwapo...Chiv 2:17ayimba nyimbo yatsopano...Chiv 5:9m’mwamba mwatsopano ndi...Chiv 21:1zonse zikhale zatsopano...Chiv 21:5

TSUKA (wash)utsuke mtima wako kuchotsa...Yer 4:14[onaninso: samba, sambitsa, sambitsidwa]

TSUKA (washed)natsuka mikwingwirima yao...Mac 16:33[onaninso: chapa, konkha, masula, sambitsa, sambitsidwa]

TSUTSA (condemn)ndidzati kwa Mulungu, musanditsutse...Yoh 10:2inenso sindikutsutsa iwe...Yoh 8:11momwemo udzitsutsa iwe wekha...Aro 2:1mwa Yesu Khristu alibe kutsutsika...Aro 8:1natsutsa uchimo m’thupi...Aro 8:3ndani adzawatsutsa...Aro 8:34m’mene monse mtima wathu utitsutsa...1 Yoh 3:20mtima wathu ukapanda kutitsutsa...1 Yoh 3:21[onaninso: langa, weruza]

TSUTSA (condemned)natsutsa uchimo mthupi...Aro 8:3[onaninso: tsutsidwa, weruzidwa]

TSUTSA (convict)ndipo atadza iyeyo adzatsutsa...Yoh 16:8ndikutsutsa otsutsana naye...Tit 1:9ndikutsutsa osapembedza onse...Yuda 15

TSUTSA (convicts)ndani mwa inu anditsutsa ine...Yoh 8:46

TSUTSANA (against)lidzakhala lotsutsana...Gen 16:12nkhope yanga idzatsutsana...Lev 20:3ndiye kuti ndi wotsutsana...Mat 12:25kutsutsana ndi ambuye...Mac 4:26chilamulo chitsutsana...Agal 3:21kotsutsana ndi iwe...Chiv 2:20[onaninso: limbana, ukira]

TSUTSANA (contend)mundidziwitse chifukwa chakutsutsana...Yob 10:2anthu anatsutsana ndi mose...Eks 17:2[onaninso: kangana, limbana]

TSUTSANA (contrary)mwa njira zotsutsana ndi malamulo...Mac 18:13thupi lilakalaka potsutsana naye...Agal 5:17natsutsana nawo anthu onse...1 Ates 2:15kena kakutsutsana nacho chiphunzitso...1 Tim 1:10

TSUTSANA (controversy)kapena zakutsutsana...Deut 17:8adzatsutsana ndi anthu onse...Yer 25:31

TSUTSANA (plead)adzatsutsana ndi anthu onse...Yer 25:31[onaninso: nenera, pemphera, pemphero,weruza]

TSUTSIDWA (condemned)ndi mau ako omwe udzatsutsidwa...Mat 12:37[onaninso: tsutsa, weruzidwa]

TUBALA-KAINI (Tubal-Cain)mwana wa Lameki...Gen 4:19-22

TUBALA (Tubal)mwana wa Yafeti...Gen 10:2— fuko lomwe linali limodzi ndi Yavani ndi Meseki...Yes66:19anali kugulu la nkhondo la Gogi...Ezek 38:2,3chilango chake...Ezek 32:26,27

TUKULA (lift)titukulire mitima yathu...Mali 3:41[onaninso: kweza]

TUKULIDWA (lofty)amene ali wamtali wotukulidwa...Yes. 57:15[onaninso: kweza, kwezeka]

TULO (sleep)adagonetsa Adamu tulo...Gen 2:21anthu anagona tulo...Yob 4:13kuti ndingagone tulo...Mas 13:3mudawagonetsa tulo...Mas 76:5kuti ndikhale m’tulo...Mas 132:4udzakhala ndi tulo...Miy 3:24usakondetse tulo...Miy 20:13chuma sichigonetsa tulo...Mlal 5:12wakugonetsa tulo...Yes 29:10ndafanato tulo...Dan 8:18dzuka wa m’tulo...Aef 5:14tisagone tulo...1 Ates 5:6[onaninso: gona]

TULO (sleeps)ali mtulo chabe...Mat 9:24wagona tulo...Yoh 11:11ndimapeza tulo...Mas 3:5[onaninso: gona]

TULUKA (arise)

Page 152: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

adzakutulukirani...Yes 60:2lidzakutulukirani...Mal 4:2[onaninso: nyamuka, uka]

TUMA (send)Mulungu adzatumiza chifundo...Mas 57:3“kodi ndidzatuma yani”...Yes 6:8adzatuma mpulumutsi...Yes 19:20ndikutumani ngati nkhosa...Mat 10:16adzatuma angelo ake...Mat 13:41“Tumani Lazaro aviike...Luk 16:24amene Atate adzamtuma...Yoh 14:26Monga Atate adandituma...Yoh 20:21

TUMA (sent)Mzimu wao, ndipo wandituma...Yes 48:18sindidawatume ndine...Yer 23:21monga Atate wandituma...Yoh 20:21ngati palibe wowatuma...Aro 10:15ndipo anatuma Mwana wake...1 Yoh 4:10

TUMIKIRA (serve)ndi kutumikira Iyeyu...Deut 6:13kumatumikira Mulungu...Yer 5:19ndi kumamtumikira...Zef 3:9kutumikira mabwana awiri...Mat 6:24kuti ena adzamtumikira...Mat 20:28ndimatumikira malamulo...Aro 7:25kwenikweni mudzitumikirana...Agal 5:13Ambuye amene mukuwatumikira...Akol 3:24kukatumikira Mulungu wamoyo...Aheb 9:14amtumikira Iye usana nsi usiku...Chiv 7:15

TUMIKIRA (service)kutumikiraku muli nako nkutani...Eks 12:26kuti akutumikira Mulungu...Yoh 16:2achangu mumzimu, tumikirani Ambuye...Aro 12:11

TUMIKIRA (serving)mwanayo natumikira Yehova...1 Sam 2:11zikwizikwi namtumikira...Dan 7:10pa kutumikira Ambuye iwowa...Mac 13:2zosiyanasiyana zotumikira...1 Akor 12:5wina akatumikira, achite...1 Pet 4:11

TURUKA (creep)pamenepo zituruka zirombo zonse...Mas 104:20[onaninso: kwawa]

TURUTSA (drive)nayamba kuturutsa akugulitsa...Marko 11:15[onaninso: pirikitsa]

TURUTSA (drove)naturutsira kunja onse...Mat 21:12anaturutsa onse m’Kachisimo...Yoh 2:15[onaninso: pirikitsa]

U

UBATIZO (baptism)akudza ku ubatizo wake...Mat 3:7ubatizo wa Yohane uchokera...Mat 21:25koma ndili ndi ubatizo...Luk 12:50mu ubatizo wa Yohane...Mac 19:3mwa ubatizo kulowa mu imfa...Aro 6:4chikhulupiriro chimodzi, ubatizo umodzi...Aef 4:5pamodzi ndi Iye mu ubatizo...Akol 2:12ndicho ubatizo...1 Pet 3:21chiphunzitso cha ubatizo...Aheb 6:2

UBWENZI (acquaintances) adaali abwenzi...Yer 20:10

UBWINO (advantage)kuchimwa kwanga ubwino...Yob 35:3mkwabwino kuti...Yoh 16:7[onaninso: chenjera]

UBWINO (goodness)ndikaone ubwino wa Yehova...Mas 27:13kulemera kwa ubwino wake...Aro 2:4[onaninso: ukoma]

UCHI (honey)chozuna kuposa uchi...Ower 14:18ndikadakukhutitsani ndi uchi...Mas 81:16uzidya uchi poti ndiwambiri...Miy 24:13kwabwino kudya uchi wambiri...Miy 25:27kuli ngati uchi ndi mkaka...Nyi 4:11chinali dzombe ndi uchi...Mat 3:4

UCHIMO (sin)ndidabadwa mu uchimo...Mas 51:5uchimo umachititsa...Miy 14:34uchimo udalowa mdziko...Aro 5:12uchimo udaalipo padziko...Aro 5:13tidzingokhala mu uchimo...Aro 6:1kufa kulekana ndi uchimo...Aro 6:10uchimo sudzakhalanso ndi...Aro 6:14uchimo ndiwo udandipha...Aro 7:13koma uchimo umene...Aro 7:17Iye adatsuka uchimo...Aro 8:3kuti achotse uchimo...Aheb 9:26pathupi nkubala uchimo...Yak 1:15[onaninso: chimwa, tchimo]

UCHITSIRU (folly)uchitsiru umakondweretsa...Miy 15:21uchitsiru umabweretsa chilango...Miy 16:22utsiru ukhazikika pamwamba...Mlal 10:6[onaninso: zopusa]

UDANI (enmity)ndipo ndidzaika udani...Gen 3:15chisamaliro cha thupi chidana...Aro 8:7atachotsa udani mthupi lake...Aef 2:15atapha nao udaniwo...Aef 2:16ubwenzi wa dziko lapansi ndi udani...Yak 4:4

UDANI (wrath)wokhala nao udani waukulu...Chiv 12:12[onaninso: kuzaza, kwiya, mkwiyo, ukali]

UDINDO (office)wina alandire udindo...Mas 109:8

UDZU (grass)ananga udzu wakuthengo...2 Maf 19:26zidzachuluka ngati udzu...Yob 5:25ali ngati udzu wongotsitsimuka...Mas 90:5masiku ake sakhalitsa, ali ngati a udzu...Mas 103:15udzu umauma, maluwa amafota...Yes 40:7amaveka motere udzu wakuthengo...Mat 6:30udzu umauma ndipo duwa limathothoka...1 Pet 1:24

UFULU (grace)koma Nowa anapeza ufulu pamaso pa Yehova...Gen 6:8[onaninso: chisomo]

UFULU (liberty)m’dzikomo kuti akhale aufulu...Lev 25:10ndipo ndidzayenda mwaufulu...Mas 119:45akapolo kuti adzalandira ufulu...Yes 61:1wandituma kuti ndikawapatse ufulu...Luk 4:18

Page 153: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi kulandirako ufulu ndi ulemelero...Aro 8:21kodi ufulu wanga utsekerezedwa...1 Akor 10:29kumene kuli Mzimu wa Ambuye kuli ufulu...2 Akor 3:17adatimasula kuti tikhale mfulu...Agal 5:1adakuitanani kuti mukhale mfulu...Agal 5:13angwiro komanso opatsa ufulu...Yak 1:25inde mudzikhala ngati mfulu...1 Pet 2:16

UKA (arise)ndiuka tsopano ati Yehova...Mas 12:5ukani tithandizeni...Mas 44:26auke mulungu...Mas 68:1pamene ndidzauka...Mas 17:15ndidzauka ndekha m’mamawa...Mas 108:2mthaka ya fumbi adzauka...Dan 12:2sanauke wakubadwa mwa akazi...Mat 11:11nthawi yabwino yakuuka...Aro 13:11[onaninso: nyamuka, tuluka]

UKA (awake)maonekedwe anu pamene ndidzauka...Mas 17:15ogona m’fumbi lapansi adzauka...Dan 12:2nthawi yabwino yakuuka kutulo...Aro 13:11ukani molungama...1 Akor 15:34[onaninso: dikira, galamuka, khala maso, kumika]

UKA (resurrection)iwo amati akufa sadzauka...Mat 22:23chifukwa chake m’kuuka kwa akufa...Mat 22:28adzauka kuti akhale ndi moyo...Yoh 5:29woukitsa anthu akufa...Yoh 11:25za kuuka kwa akufa...Mac 17:18adzauka kwa akufa...Mac 24:15pa kuuka kwa akufa...Aro 6:5anthu akufa sadzaukanso...1 Akor 15:12ndi mphamvu ya kuuka kwake...Afil 3:10kuuka kwa akufa kudachitika...2 Tim 2:18kudzaukanso ndi moyo...Aheb 11:35kumeneku ndiye kuuka...Chiv 20:5

UKA (risen)Ambuye adaukadi...Luk 24:34amene adauka kwa akufa...Aro 8:34ngati akufa sadzauka...1 Akor 15:13kuti Khristunso sadauke...1 Akor 15:13ngati Khristu sadauka...1 Akor 15:17Khristu adauka ndithu...1 Akor 15:20kosi kuuka kwa akufa...Marko 9:10

UKA (stand)ndidzauka potsiriza pa fumbi...Yob 19:25adzandiukira ndani kutsutsana nao ochita...Mas 94:16[onaninso: chirimika, ima, khala, khazikika, limba,

tsimikizidwa]

UKALI (fierceness)mphesa mwa vinyo waukali wa mkwiyo...Chiv 19:15[onaninso: kuopsa]

UKALI (furious)madzudzulo aukali...Ezek 5:15wobwezera chilango ndi waukali ndithu...Nah 1:2[onaninso: kwiya, laswa mtima]

UKALI (fury)ndilibe ukali, ndani adzalimbanitsa...Yes 27:4adzala ndi ukali wa Yehova...Yes 51:20Iye adzabwezera amaliwongo ake ukali...Yes 59:18ndi ukali wanga unandichirikiza ine...Yes 63:5ndi mkupsa mtima ndi m’ukali...Yer 21:5ndidzakhutitsa ukali wanga pa iwo...Ezek 5:13ndidzawakwaniritsa ukali wanga...Ezek 6:12

osamvera chilango mumkwiyo wa ukali...Mik 5:15

UKALI (wrath)munthu waukali alipire mwini...Miy 19:19[onaninso: kuzaza, kwiya, mkwiyo, udani]

UKAPOLO (bondage)chifukwa cha ukapolo….Eks 2:23m’nyumba ya akapolo...Eks 13:14sinalandira mzimu wa ukapolo...Aro 8:15kuti akachititse ukapolo...Agal 4:24akubalira ukapolo...Agal 2:4adamangidwa ukapolo...Aheb 2:15musakodwenso ndi goli la ukapolo...Aheb 5:1ameneyo adzakhalanso kapolo...2 Pet 2:19

UKAPOLO (captivity)Mulungu wanu adzauchotsa ukapolo...Deut 30:3Ayuda apita ku ukapolo...Malio 1:3nthawi imene Aisraeli anatengedwa ukapolo...Mat 1:17landitsandutsa kapolo...Aro 7:23kutengedwa ku ukapolo...Chiv 13:10[onaninso: kugonjetsa, undende]

UKIRA (against)ukayamba kuukira...Mat 12:25mtundu ulionse udzaukirana...Mat 24:7ndiye adandiukira...Yoh 13:18[onaninso: limbana, tsutsana]

UKIRA (rebel)mukuti muukire mfumu...Neh 2:19[onaninso: galukira, panduka, pikisana]

UKIRA (rebellion)amangofuna zoukira...Miy 17:11zidachitikira pomuukira Mulungu...Aheb 3:8chifukwa cha kuukira Mulungu...Yuda 11[onaninso: galukira, pandukira]

UKIRA (rebellious)anthu oukira asadzikweze...Mas 66:7anthu oukira amawapirikitsira...Mas 68:6atsogoleri ao onse andiukira...Hos 9:15[onaninso: pandukira]

UKOMA (goodness)ndidzapititsa ukoma wanga...Eks 33:19ndi wa ukoma mtima wochuluka...Eks 34:6ukoma ndi chifundo zidzanditsata...Mas 23:6kukoma kwanu ndiko kwakukuru...Mas 31:19ukoma wake ndiwaukulu ndithu...Zek 9:17chifundo, kukoma mtima...Agal 5:22[onaninso: ubwino]

UKONDE (net)nandizinga ndi ukonde...Yob 19:6anatchera ukonde wao...Mas 35:7ananditchera ukonde apo...Mas 57:6monga nswala muukonde...Yes 51:20azigwira muukonde wake...Hab 1:15[onaninso: khoka]

UKULU (abundance)chifukwa cha ukulu oposa wa mavumburutso...2 Akor 12:7[onaninso: chuluka, chuma, mphamvu, sefukira, yambiri,

zonona]

UKULU (birthright)tigulane lero ukulu wako...Gen 25:31chomwecho Esau ananyoza ukulu...Gen 25:34pamaso pa oyamba monga ukulu wake...Gen 43:33

Page 154: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

amene anagulitsa ukulu wake...Aheb 12:16

UKULU (exaltation)okondwerera ndi ukulu wanga...Yes 13:3adzitamandire pa ukulu wache...Yak 1:9[onaninso: kuza]

UKULU (greatness)ndipo ndi ukulu wanu waukulu...Eks 15:7monga mwa mphamvu yanu yaikulu...Mas 79:11ndi ukulu wake ngwosasanthulika...Mas 145:3ndi ukulu wanu ndidzaufotokozera...Mas 145:6nayenda mu ukulu wamphamvu...Yes 63:1ukulu woposa wamphamvu yake...Aef 1:19

UKULU (magesty)Mulungu ali nao ukulu...Yob 37:22ulemelero wa ukulu...Mas 145:5padzanja lamanja la ukulu...Aheb 1:3koma tinapenya m’maso ukulu...2 Pet 1:16zikhale ulemelero, ukulu, mphamvu...Yuda 25

UKWATI (marry)akuletsa ukwati...1 Tim 4:3[onaninso: kwatira, kwatiwa]

UKWATI (wedding)kukaitana oitanidwa ku ukwati...Mat 22:3idzani ku ukwati...Mat 22:4kuno kuphwando la ukwati...Mat 22:9analowa naye pamodzi muukwati...Mat 25:10tsiku lachitatu panali ukwati...Yoh 2:1

ULAI (Ulai)malo omwe Daniele anaona masomphenya...Dan 8:2-16

ULAMULIRO (authorities)kumeneko angelo ndi maulamuliro...1 Pet 3:22[onaninso: olamulira]

ULAMULIRO (authority)adalemba ndi ulamuliro onse...Est 9:29ankawaphunzitsa monga munthu waulamuliro...Mat 7:29ndidzakupatsani ulamuliro...Luk 4:6amene ali ndi ulamuliro...1 Tim 2:2uzichita zimenezi ndi ulamuliro...Tit 2:15[onaninso: mphamvu, olamulira]

ULAMULIRO (dominion)alamulire pa nsomba...Gen 1:26Mulungu ali ndi ulamuliro wonse...Yob 25:2mudampatsa ulamuliro...Mas 8:6ulamuliro udzakhala m’manja mwake...Yes 9:6tikulamulidwa ndi ena...Yes 26:13ndiko kulamulira kosatha...Dan 4:34mphamvu ndi ulamuliro...Yuda 25[onaninso: chita ufumu]

ULEMELERO (beauty)ulemelero wako Israyeli...2 Sam 1:19[onaninso: chisomo, koma, kongoletsa, kukongola]

ULEMELERO (glory)ndionetsenitu ulemelero wanu...Eks 33:18nati ulemelero wachoka kwa Israeli...1 Sam 4:21ulemelero wanga ndi wondiweramitsa...Mas 3:3munaika ulemelero wanu pa thambo...Mas 8 :1mfumu imene ya ulemelero ndani...Mas 24:8malo akukhalamo ulemelero...Mas 26:8mphamvu yanu ndi ulemelero wanu...Mas 63:2adzanenera ulemelero wa ufumu...Mas 145:11ulemelero wa anyamata ndiwo...Miy 20:29kubisa kanthu ndi ulemelero wa Mulungu...Miy 25:2

ulemelero wanga ine sindidzapereka...Yes 60:2ulemelero wake udzaoneka pa iwe...Yes 60:2ufanana ndi yani mu ulemelero ndi...Ezek 31:18ndidzasanduliza ulemelero mkati mwake...Zek 2:5Yehova, nadzasenza ulemelerowo...Zek 6:13pakuti ufumu, mphamvu ndi ulemelero...Mat 6:13angakhale Solomo mu ulemelero wake...Mat 6:29mwana wa munthu adzabwera mu ulemelero...Mat 16:27ndi mphamvu ndi ulemelero waukulu...Mat 24:80ulemelero ukhale kwa Mulungu...Luk 2:14ndipo tinaona ulemelero wake...Yoh 1:14m’Galileya naonetsa ulemelero...Yoh 2:11koma ine sinditsata ulemelero wanga...Yoh 8:50ulemelero umene ndili nao ndi inu...Yoh 17:5ulemelero umene mwandipatsa ine...Yoh 17:22chifukwa sanapata Mulungu ulemelero...Mac 12:23iwo amene akufunafuna ulemelero...Aro 2:7naperewera pa ulemelero wa Mulungu...Aro 3:23ali nawo umwana ndi ulemelero...Aro 9:4akadziwitse ulemelero wake waukulu...Aro 9:23ukhale ulemelero kunthawi zonse...Aro 16:27mkazi ali ulemelero wa mwamuna...1 Akor 11:7chifukwa cha ulemelero woposawo...2 Akor 3:10uthenga wabwino wa ulemelero wa Khristu...2 Akor 4:4kwakukulu ndi kosatha kwa ulemelero...2 Akor 4:17monga mwa chuma chake mu ulemelero...Afil 4:19mudzaonekera pamodzi ndi Iye mu ulemelero...Akol 3:4inu ndinu ulemelero wathu ndi...1 Ates 2:20pakutenga ana ambiri alowe ulemelero...Aheb 2:10ulemelero wao onse ngati duwa...1 Pet 1:24amene ali nao ulemelero ndi mphamvu...1 Pet 4:11Mzimu wa ulemelero ndi Mzimu wa Mulungu...1 Pet 4:14kukuimikani pamaso pa ulemelero...Yuda 24kulandira ulemelero ndi ulemu...Chiv 4:11ulemelero wa Mulungu uunikira...Chiv 21:23

ULEMU (honour)adakupatsa, ndipo chuma ndi ulemu...1 Maf 3:13ikondwera kumchitira ulemu...Est 6:6naukhalitse ulemu wanga...Mas 7:5munthu wa ulemu koma...Mas 49:20ndi kumchitira ulemu...Mas 91:15pamaso pake pali ulemu...Mas 96:6ulemu wa okondedwa ake...Mas 149:9chifatso chotsogolera ulemu...Miy 15:33momwemo ulemu suyenera...Miy 26:1atate uli kuti ulemu...Malaki 1:6mneneri sakhala opanda ulemu...Mat 13:57ulemu sandiulandira kwa anthu...Yoh 5:41Atate adzamchitira ulemu...Yoh 12:26chotengera chimodzi cha ulemu...Aro 9:21a kuwaopa; ulemu kwa eni...Aro 13:7tiziyesa zochepa ulemu...1 Akor 12:23m’chiyeretso ndi ulemu...1 Ates 4:4ukhale ulemu ndi ulemelero...1 Tim 1:17ayesedwe oyenera ulemu...1 Tim 5:17ndipo zina za ulemu...2 Tim 2:20adzitengera ulemuwo...Aheb 5:4chitirani mfumu ulemu...1 Pet 2:17kwa Mulungu Atate ulemu...2 Pet 1:17zipereka ulemelero ndi ulemu...Chiv 4:9[onaninso: lemekeza]

ULEMU (honourable)anthu amchitira ulemu...1 Sam 9:6chochita iye nchaulemu...Mas 111:3kuli ulemu kwa mwamuna...Miy 20:3[onaninso: lemekezeka]

ULESI (laziness)ulesi ugonetsa tulo...Miy 19:15nyumba nidontha ndi ulesi...Mlal 10:18

Page 155: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ULESI (lazy)koma aulesi adzakhala...Miy 12:24munthu waulesi sapedza...Miy 12:27munthu waulesi amakhumbira...Miy 13:4waulesi amati akapisa dzanja...Miy 19:24munda wa munthu wa ulesi...Miy 24:30waulesi amadziyesa wanzeru...Miy 26:16zilombo zoipa, aulesi...Tit 1:12

ULUKA (fly)bwenzi nditauluka...Mas 55:6nkuyamba kuuluka kunka...Miy 23:5

ULULA (reveal)zamumlengalenga zidzaulula...Yob 20:27[onaninso: ululira, vumbulutsa]

ULULA (revealed)Mulungu wathu sanatiululire...Deut 29:29zimene adandiululira...2 Akor 12:1[onaninso: onetsa, onetsedwa, onetsera, vumbulutsa,vumbulutsidwa]

ULULIRA (reveal)ndidzawaululira iwo kuchuruka...Yer 33:6mwanayo afuna kumuululira...Mat 11:27adatsimikiza zondiululira...Agal 1:16[onaninso: ulula, vumbulutsa]

ULULU (poison)muli ululu wa mamba...Mas 140:3ululu wake wonga wa...Aro 3:13lodzaza ndi ululu wakupha...Yak 3:8

ULULU (pained)mtima wanga ukumva ululu...Mas 55:4[onaninso: zowawa]

ULULU (pains)ndamva nazo ululu...Yes 21:3[onaninso: zowawa]

UMA (barren)koma Sarai anali wouma; analibe mwana...Gen 11:30yimba iwe wouma, amene sunabala...Yes 54:1odala ali ouma ndi mimba yosabala...Luk 23:29[onaninso: chumba, kusabala, opanda zipatso, wosaona

mwana]

UMA (dried)mphamvu yanga yauma ngati mphale...Mas 22:15adaona mkuyu uja waumiratu...Marko 11:20[onaninso: iphwa]

UMA (dry)paubweya pokha panali pouma...Owe 6:40nanga mtengo wouma ndiye...Luk 23:31[onaninso: umitsa]

UMBA (formed)Yehova Mulungu anaumba...Gen 2:7manja ake anaumba...Mas 95:5munandiumba ndisanabadwe...Mas 139:13kufikira Khristu aumbika...Agal 4:19[onaninso: lenga]

UMBOMBO (greediness)chidetso chonse mu umbombo...Aef 4:19

UMBONI (tesimony)

a umboni wonama...Malak 3:5yonse apezepo umboni...Mat 24:14timachitira umboni...Yoh 3:11ndidzichitira ndekha umboni...Yoh 5:31ine ndili ndi umboni...Yoh 5:36

UMBONI (witness)a umboni onama...Malak 3:5wina ondichitira umboni...Yoh 5:32ankachitira umboni mau...Mac 14:3udzachitira umboni kwa...Mac 22:15Mulungu akundichira umboni...Afil 1:8atatu kwa ochitira umboni...1 Yoh 5:7timalandira umboni wa anthu...1 Yoh 5:9[onaninso: mboni]

UMBONI (witnessed)aneneri omwe amachitira umboni...Aro 3:21amene popereka umboni...1 Tim 6:13

UMIRIRA (defend)komanso ndidzaumirira mayendedwe anga pamaso pake...Yob13:15[onaninso: chinjiriza, teteza]

UMIRIRA (dictates)amaumirira kutsata zofuna...Yer 23:17

UMIRIZA (compel)nuwaumirize anthu alowe...Luk 14:23[onaninso: kakamiza]

UMIRIZA (entreat)musandiumirize kuti ndikusiyeni...Rut 1:16[onaninso: pempha]

UMITSA KHOSI (stiff necked)musati muumitse makosi...2 Mbir 30:8ouma khosi ndi osadulidwa...Mac 7:51

UMITSA (dry)pompo Yehova adaumitsa nyanja...Eks 14:21ndidzaumitsa nyanja ya Babiloni...Yer 51:36ndimaumitsa mitengo...Ezek 17:24ndidzaumitsa mtsinje wa Nairo...Ezek 30:12[onaninso: uma]

UMODZI (unity)anthu akakhala amodzi...Mas 133:1kusunga umodzi mwa Mzimu...Aef 4:3tidzafika ku umodzi...Aef 4:13

UMPHAWI (poverty)umphawi wa anthu osauka...Miy 10:14umphawi ndi manyazi...Miy 13:18kumabweretsa umphawi...Miy 14:23ungagwe mu umphawi...Miy 20:13musandipatse umphawi...Miy 30:10mwa umphawi wake...Luk 21:4kuti ndi umphawi wakewo...2 Akor 8:9ndiponso umphawi wanu...Chiv. 2:9[onaninso: kusauka]

UMULUNGU (godhead)nzosatha ndiponso umulungu wake...Aro 1:20umulungu wonse umakhalamo wathunthu...Akol 2:9

UMWANA (adoption)mzimu wa umwana...Aro 8:15kulindirira umwana...Aro 8:23ali nao umwana...Aro 9:4tikalandire umwana...Agal 4:5

Page 156: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ngati ana...Aef 1:5

UMWANA (childhood)pakuti ubwana ndi unyamata...Mlal 11:10zidamyamba ali mwana...Marko 9:21kuyambira ukali mwana...2 Tim 3:15

UNAMWALI (flower)ngati pali kupitirira pa unamwali wake...1 Akor 7:36[onaninso: duwa]

UNDENDE (captivity)munapita tao undende...Mas 68:18anamanga ndende undende...Aef 4:8[onaninso: kugonjetsa, ukapolo]

UNGWIRO (integrity)ndi mtima wanga wangwiro...Gen 20:5munthu wangwiro ndi woongoka...Yob 2:3naumirirabe kukhala wangwiro...Yob 2:3kuti Mulungu adziwe ungwiro wanga...Yob 31:6pakuti ndayenda muungwiro wanga...Mas 26:1mugwirizize muungwiro wanga...Mas 41:12

UNIKIDWA (illuminated)mutaunikidwa mudapirira...Aheb 10:32dziko linaunikidwa ndi ulemerero...Chiv 18:1[onaninso: unikira]

UNIKIRA (illuminated)ulemerero wa Mulungu uunikira...Chiv 21:23[onaninso: unikidwa]

UNIKIRA (light)younikira pokhala poyera...Yob 38:19Mulungu amene amatiunikira...Mas 118:27monga nyali younikira...2 Pet 1:19[onaninso: kuunika, kuwala, unikira]

UNSEMBE (priesthood)adaipitsira unsembe wao...Neh 13:29kusintha pa unsembe...Aheb 7:12motero unsembe wake...Aheb 7:24[onaninso: ansembe]

UNYAMATA (youth)anali mnyamata chabe...1 Sam 17:42machimo a unyamata wanga...Mas 25:7muzikondwerera unyamata...Mlal 11:9manyazi pa unyamata wako...Yes 54:4poona kuti ndiwe wachinyamata...1 Tim 4:12zilakolako zoipa zachinyamata...2 Tim 2:22

UNYINJI (company)ndi kwa unyinji wochuluka...Aheb 12:22[onaninso: khamu, mayanjano]

UNYINJI (crowd)usatsata unyinji...Eks 23:2

UNYOLO (chain)walemeretsa unyolo wanga...Malio 3:7phompho ndi unyolo waukulu...Chiv 20:1

UPHUNGU (counsel)uphungu ndi luntha...Yob 12:13uphungu wa oipa unditalikira...Yob 21:16uphungu wa Mulungu unakhala...Yob 29:4ndani uyu adetsa uphungu...Yob 38:2wosayenda mu uphungu wa oipa...Mas 1:1mudzanditsogolera ndi uphungu...Mas 73:24munapeputsa uphungu wanga...Miy 1:25

anakana uphungu wanga...Miy 1:30pochuluka uphungu pali chipulumutso...Miy 11:14uphungu wa m’mtima mwa munthu...Miy 20:5uphungu utsimikiza zolingalira...Miy 20:18mwa uphungu wa chifuniro chake...Aef 1:11

URI WA KU KALDEYA (Ur of the Chaldeans)mzinda womwe Abramu anakulira...Gen 11:28-31, 15:7woikidwa ku Mesopotamiya ndi Stefano...Mac 7:2-4

URIMU (Urim)wotchedwa Urimu ndi...Eks 28:30Tumimu ndi Urimu...Deut 33:8

URIYA (Uriah)mhiti wa fuko la Ahiti, mmodzi wa ankhondo a Davide...2Sam 23:39wamkulu wansembe nthawi ya Ahazi...2 Maf 16:10-16mneneri nthawi ya Yeremiya...Yer 26:20-23

USANA (day)anatcha kuyerako usana...Gen 1:5usana ndi usiku sizidzaleka...Gen 8:22usana ndi usiku uchulukitsa mau...Mas 19:2dzuwa silidzaomba usana...Mas 121:6usiku uwala ngati usana...Mas 139:12pokhala pa usana...Yoh 9:4ndi ana a usana...1 Ates 5:5[onaninso: tsiku]

USIKU (night)mdimao anautcha usiku...Gen 1:5ndiwo usiku wosungira Yehova...Eks 12:42mtambo wamoto usiku...Eks 13:22koma usiku undikulira...Yob 7:4wakupatsa nyimbo usiku...Yob 35:10usiku uonetsa nzeru...Mas 19:2malonda a usiku...Mas 119:148nyenyezi ziweruza usiku...Mas 136:9moyo wanga ndinakhumba usiku...Yes 26:9umene unamera usiku...Yon 4:10nachezera usiku wonse...Luk 6:12anadza kwa Yesu usiku...Yoh 3:2ukudza usiku pamene palibe...Yoh 9:4amene anadza kwa iye usiku...Yoh 19:39usiku wapita, ndi dzuwa...Aro 13:12lidzadza monga mbala usiku...1 Ates 5:2a usana, sitiri a usiku...1 Ates 5:5pakuti sipadzakhala usiku...Chiv 21:25ndipo sikukdzakhalanso usiku...Chiv 22:5

USIWA (nakedness)njala kapena usiwa...Aro 8:35[onaninso: maliseche]

UTA (bow)uta wake unakhala wamphamvu...Gen 49:24uta wanga udzakhala wosalifuka...Yob 29:20sinditama uta wanga...Mas 44:6athyola uta...Mas 78:57anapatuka ngati uta...Mas 78:57osawapulumutsa ndi uta...Hos 1:7womkwerayo anali nao uta...Chiv 6:2[onaninso: gwada, werama]

UTALI (height)ndipo penyani kutalika kwake...Yob 22:12ngakhale utali, ngakhale kuya...Aro 8:39kupingasa ndi utali...Aef 3:18

UTAWALEZA (rainbow)ndikuika utawaleza m’mitambo...Gen 9:13

Page 157: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

wachifumuwo panali utawaleza...Chiv 4:3

UTHENGA WABWINO (Gospel)uwu ndi uthenga wabwino...Marko 1:1khulupirirani uthenga wabwino...Marko 1:15uthenga wabwino uyenera uyambe...Marko 13:10kuchitira umboni uthenga wabwino...Mac 20:24kukanena uthenga wabwino...Aro 1:9uthenga wabwino sundichititsa manyazi...Aro 1:16amene alalikira uthenga wabwino...1 Akor 9:14ngati uthenga wabwino wathu uphimbika...2 Akor 4:3kutsata uthenga wabwino wina...Agal 1:6uthenga wabwino wachipulumutso...Aef 1:13chinsinsicho cha uthenga wabwino...Aef 6:19chiyembekezo cha uthenga wabwino...Akol 1:23wakukhala nao uthenga wabwino...Chiv 14:6

UTHENGA (message)ndamva uthenga wochokera kwa...Yer 49:14[onaninso: mau]

UTSI (smoke)ngati utsi wotuluka...Gen 19:28mphepo imachitira utsi...Mas 68:2amangopita ngati utsi...Mas 102:3chipululucho ngati utsi...Nyi 3:6utsi udzafuka kosalekeza...Yes 34:10udzazimirira ngati utsi...Yes 51:6magazi, moto ndi utsi...Mac 2:19padatuluka utsi...Chiv 9:2mudaadzaza utsi...Chiv 15:8utsi wamzindawo...Chiv 19:3

UTSIRU (futility)pakuti cholengedwacho chagonjetsedwa kuutsiru...Aro 8:20[onaninso: chabe, panda pake]

UTUMIKI (ministry)amitundu, ndilemekeza utumiki...Aro11:13ngati utumiki wa imfa wolembedwa...2 Akor 3:7tiri nao utumiki umene, monga...2 Akor 4:1natipatsa utumiki wa chiyanjanitso...2 Akor 5:18mtima ku ntchito ya utumiki...Aef 4:12samalira utumiki umene...Akol 4:17wabwino, kwaniritsa utumiki...2 Tim 4:5Iye walandira chitumikiro...Aheb 8:6

UTUMWI (apostleship)utumiki uwu ndi utumwi...Mac 1:25chisomo ndi utumwi...Aro 1:5chizindikiro cha utumwi...1 Akor 9:2pomutuma ngati mtumwi...Agal 2:8

UZA (command)mundiuze ndidze kwa Inu...Mat 14:28mufuna kuti ife tiuze moto...Luk 9:54[onaninso: lamula, mau]

UZA (Uzzah)mwana wa Abinadabu, anakanthidwa atakhudza likasa laChipangano...2 Sam 6:3-11

UZIMU (spiritual)amene ali wauzimu...1 Akor 2:15monga ndi auzimu...1 Akor 3:1kapena wauzimu...1 Akor 14:37chauzimu sichiri choyamba...1 Akor 14:46inu auzimu mubweze...Agal 6:1

UZIRA (inspiration)

mochita ngati kuwauzira...2 Tim 3:16

UZIYA (Uzziah)mfumu ya Yuda, wotchedwanso Azariya...2 Maf 14:24, 15:1-7analamulira molungama...2 Mbir 26:1-15anasokoneza mwambo wa ansembe, anakanthidwa ndikhate...2 Mbir 26:16-21za moyo wake zinalembedwa ndi Yesaya...2 Mbir 26:22,23

V

VALA (arrayed)ulemerero wake wonse sanavala...Mat 6:29ovala zovala zoyera ndiwo ayani?...Chiv 7:13ndipo mkazi anavala...Chiv 17:4

VALA (clothed)banja lake lonse livala...Miy 31:21munthu wovala zofewa...Mat 11:8wovala ndi wanzeru zake...Marko 5:15amavala chibakuwa ndi nsalu...Luk 16:19avala chovala chowazidwa mwazi...Chiv 19:13[onaninso: veka, vekedwa]

VEKA (clothe)ndi kuwaveka malaya...Eks 40:14mundiveka khungu ndi mnofu...Yob 10:11ansembe ake ndidzawaveka...Mas 132:16ndidzawaveka adani ake...Mas 132:18ngakhale uziveka ndi zofiira...Yer 4:30ngati Mulungu aveka chotero...Mat 6:30

VEKA (clothed)maraya azikopa nawaveka iwo...Gen 3:21wamveka pakhosi pake...Yob 39:19ndipo munandiveka chikondwerero...Mas 30:11wandiveka ndi ukuru...Mas 93:1anavalanso temberero...Mas 109:18ansembe anu avale chilungamo...Mas 132:9ndinakuvekanso ndi nsalu...Ezek 16:10kuti ukadziveke kuti manyazi...Chiv 3:18[onaninso: vala, vekedwa]

VEKA (crown)muveka chakachi ndi ukoma wanu...Mas 65:11[onaninso: korona]

VEKEDWA (clothed)ndikukhumbitsa kuvekedwa...2 Akor 5:2mkazi wovekedwa dzuwa...Chiv. 12:1[onaninso: vala, veka]

VIIKA (dipped)adaviika chala chake...Lev 9:9chinali choviika m’magazi...Chiv 19:13[onaninso: sunsa]

VINA (dance)ana ao amavinavina...Yob 21:11atamande dzina lake povina...Mas 149:3mphindi yakulira ndi mphindi ya kuvina...Mlal 3:4kuvina kwathu kwasanduka kulira...Mali 5:15ndipo inu simunavina...Mat 11:17ndipo Davide anavina ndi mphamvu...2 Sam 6:14mwana wamkazi wa Herodiya anavina...Mat 14:6

VINYO (wine)namwa vinyo wake naledzera...Gen 9:24ndi vinyo wokondweretsa mtima...Mas 104:15anthu okhuta vinyo...Miy 20:1ndi kufiira kwa vinyo...Miy 23:31chako nchoposa vinyo...Nyi 1:2

Page 158: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

kufikira vinyo awaledzeretsa...Yes 5:11mudzagule vinyo ndi mkaka...Yes 55:1Yesu vinyo wosasa...Mat 27:34pamene vinyo adatha...Yoh 2:3musaledzere vinyo...Aef 5:18koma uzimwako vinyo...1 Tim 5:23osakodwa nacho chikondi cha pavinyo...Tit 2:3adamwetsa chikho cha vinyo...Chiv 16:19

VOMERA (acknowledge)uzivomera kuti...Miy 3:6vomera kuti...Yer 3:13ndinavomera...Mas 32:5[onaninso: dziwa, zindikira, vomereza]

VOMERA (answers)ndalama zivomera zonse...Mlal 10:19[onaninso: bwezera, mayankho]

VOMERA (confess)ndivomera choipa changa...Mas 32:5[onaninso: vomereza]

VOMEREZA (acknowledge)wovomereza mwana...1 Yoh 2:23[onaninso: dziwa, zindikira, vomera]

VOMEREZA (agreed)munthu aliyense adzavomereza iye...Yoh 9:22wavomereza chivomerezo chabwino...1 Tim 6:12koma wakuvomereza, nawasiya...Miy 28:13iye amene avomereza kuti Yesu...1 Yoh 4:15ndi mkamwa avomereza kutengapo...Aro10:10[onaninso: pangana]

VOMEREZA (approve)avomereza mau ao...Mas 49:13ndiponso avomereza ndi iwo...Aro1:32nuvomereza zinthu zoposa...Aro2:18navomerezeka ndi anthu...Aro14:18kwa Mulungu wovomerezeka...2 Tim 2:15pamene wavomerezeka...Yak 1:12

VOMEREZA (ascribe)ndidzavomereza kuti mlengi wanga...Yob 36:2vomerezani kuti mphamvu nja Mulungu...Mas 68:34

VOMEREZA (believe)popeza sanavomereza...Marko 16:14[onaninso: khulupirira]

VOMEREZA (confess)ngati uvomereza mkamwa mwako...Aro10:9malilime onse avomereza...Aro14:11muvomerezane wina ndi mnzake...Yak 5:16ngati tivomereze machimo athu...1 Yoh 1:9ndipo ndidzavomereza dzina lake...Chiv 3:5[onaninso: vomera]

VOMEREZA (consent)wosavomerezana nawo mau amoyo...1 Tim 6:3

VOMEREZA (consented)Saulo anali kuvomerezana nao pa imfa...Mac 8:1

VOMEREZANA (agree)a inu avomerezana...Mat 18:19ndipo atatuwa amavomerezana...1 Yoh 5:8[onaninso: gwirizana]

VOMEREZETSA (commend)chakudya sichitivomerezetsa...1 Akor 8:8

VULA (lay)mutavula chinyaso...Yak 1:21[onaninso: ika, samira)

VUMBA (rain)ndidzavumbitsira iye ndi magulu...Ezek 38:22[onaninso: mvula]

VUMBULUTSA (reveal)Mulungu adzavumbulutsira inu...Afil 3:15[onaninso: ulula, ululira]

VUMBULUTSA (revealed)tsiku la kuvumbuluka Mwana...Luk 17:30monga anachivumbulutsa tsopano...Aef 3:5pa vumbulutso la Ambuye...2 Ates 1:7kutinso pa vumbulutso la...1 Pet 4:13[onaninso: onetsa, onetsedwa, onetsera, ulula, vumbulutsidwa]

VUMBULUTSIDWA (revealed)ulemelero w aYehova udzavumbulutsidwa...Yes 40:5chiri pafupi kuti chivumbulutsidwe...Yes 56:1chinsinsicho chinavumbulutsidwa...Dan 2:19ndipo pamene anavumbulutsidwa...2 Ates 2:8chokonzeka kukavumbulutsidwa...1 Pet 1:5[onaninso: onetsa, onetsedwa, onetsera, ulula, vumbulutsa]

VUNDA MTIMA (corrupt)pamodzi anavunda mtima...Mas 14:3anavunda mtima pamodzi...Mas 53:3wovunda potsata zilakolako...Aef 4:22anthu ovunditsidwa mtima...2 Tim 3:8

VUNDA (corrupted)ndipo taonani, linavunda...Gen 6:12chovunda ichi chiyenera...2 Akor 15:53simunaomboledwa ndi zovunda...1 Pet 1:18

VUNDA (corruption)simudzalola okondedwa wanu avunde...Mas 16:10[onaninso: chivundi]

VUNDIKIRA (cover)silidzavundikiranso ophedwa...Yes 26:21adzavundikira machimo aunyinji...Yak 5:20palibe kanthu kanavundikiridwa...Mat 10:26[onaninso: kuta, phimba]

VUTA (adversaries)iwo amene avuta Ayuda...Yes 11:13[onaninso: adani, otsutsana]

VUTIKA KOOPSA (agony)Yesu adavutikabe koopsa...Luk 22:44

VUTIKA (troubled)chisoni ndi kuvutika mumtima...Marko 14:33

VUTITSA (afflict)tavutitsa moyo wathu...Yes 58:3tsiku lakuvutitsa moyo...Yes 58:5chifukwa chiyani mwavutitsa ine...Num 11:11[onaninso: sautsa, zunza, zunzika]

W

WABODZA (liar)pakuti ali wabodza...Yoh 8:44wabodzayo ndani...1Yoh 2:22[onaninso: onama]

Page 159: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

WACHIGOLOLO (adulterer)diso la wachigololo...Yob 24:15

WACHIPALA (blacksmith)taona ndalenga wachipala...Yes 54:16[onaninso: m’misiri wa zitsulo]

WACHISONI (sorrowful)mkazi wa mtima wachisoni...1 Sam 1:15mtima uliwonse wachisoni...Yer 31:25anamuka wachisoni...Mat 19:22anachoka iye wachisoni...Marko 10:22[onaninso: chisoni, zisoni, zowawa]

WADAMA (fornicator)kuti munthu wina aliyense wadama...Aef 5:5wina aliyense asakhale wadama...Aheb 12:16

WAKHUNGU (blind)ndi wakhungu, ndi wausiwa...Chiv 3:17[onaninso: akhungu, khungu]

WAKUBA (thief)aliyense wakuba adzapitikitsidwa...Zek 5:3ameneyo ndi wakuba...Yoh 10:1[onaninso: mbala]

WAKUGAWIRA (arbitrator)kapena wakugawira...Luk 12:14

WAKUPHA (murderer)yense wakudana ndi mbale wake ali wakupha munthu...1 Yoh3:15[onaninso: wambanda]

WALA (brightness)a Kalonga ake anali owala...Malio 4:7ndinaona kuwala...Mac 26:13m’kuwala kumene kunali pamaso pake...2 Sam 22:13Iye ndiye kuwala koonetsa...Aheb 1:3

WALA (lights)mumawala monga momwe...Afil 2:15[onaninso: miyuni]

WALUSO (expert)ngati wankhondo waluso...Yer 50:9[onaninso: katswiri, m’misiri]

WAMANGAWA (debtor)ine ndiri wamangawa...Aro1:14

WAMBA (strike)dzuwa silidzawamba usana...Mas 121:6[onaninso: kantha, menya, panda, tentha]

WAMBANDA (murderer)iyeyo anali wambanda kuyambira pachiyambi...Yoh 8:44ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwainu...Mac 3:14asamve zowawa wina wa inu ngati wambanda...1 Pet 4:15[onaninso: wakupha]

WAMKULU (greater)Yehova ali wamkulu ndi milungu yonse...Gen 41:40Yehova ali wamkulu ndi milungu...Eks 18:11munthu wamkulu woposa Yohane...Mat 11:11kodi muli wamkulu ndi atate...Yoh 4:12kapolo sali wamkulu ndi...Yoh 13:16kapena mtumwi sali wamkulu...Yoh 13:16kapolo sali wamkulu ndi mbuye...Yoh 15:20

popeza analibe wamkulu...Aheb 6:13Mulungu ali wamkulu...1 Yoh 3:20[onaninso: posa]

WAMOYO (living)munthuyo anakhala wamoyo...Gen 2:7munthu wamoyo adandaulanji...Malio 3:39wa akufa koma wamoyo...Mat 22:32mufuniranji wamoyo pa...Luk 24:5[onaninso: amoyo]

WANJIRANJIRA (doubt)moyo wanu udzakhala wanjiranjira pamaso panu...Deut 28:66[onaninso: kayika]

WAPAKHOMO (door keeper)nkadakonda kukhala wapakhomo...Mas 84:10iyeyu wapakhomo amtsegulira...Yoh 10:3

WANSEMBE (priest)wansembe wa Mulungu...Gen 14:18ndidzasankha wansembe...1 Sam 2:35ndiwe wansembe mpaka...Mas 110:4wansembe ndi mneneri...Yes 28:7mpando wake padzakhala wansembe...Zek 6:13ndiwe wansembe mpaka muyaya...Aheb 4:14iwe ndiwe wansembe wa nthawi zonse...Aheb 5:6ndiye mkulu wa ansembe...Aheb 9:11

WANTCHITO (worker)wantchito ngwoyenera kulandira...Mat 10:10

WAWA (bitter)ndi ndiwo zowawa zamasamba...Eks 12:8ndi vinyo kwa owawa mtima...Miy 31:6amene aika zowawa m’malo...Yes 5:20musawawire mtima iwo...Akol 3:19mukamakhala nako kaduka kowawa...Yak 3:14kadzawawitsa m’mimba mwako...Chiv 10:9

WAWA (bitterly)anandichitira zowawa ndithu...Rut 1:20kulira ndi mtima wowawa...2 Maf 20:3nalira ndi kuwawa mtima...Mat 26:75

WAWA (bitterness)akufa ali nao mtima wakuwawa...Yob 21:25mtima udziwa kuwawa kwake...Miy 14:10chifukwa cha zowawa za moyo wanga...Yes 38:15ndiona kuti wagwidwa ndi ndulu yowawa...Mac 8:23ungaphuke muzu wina wakuwawa mtima...Aheb 12:15

WERAMA (bow)niweramira mtima wanga...Gen 37:7anaweramitsa miyambanso...2 Sam 22:10[onaninso: gwada, uta]

WERENGA (count)kuti akawerenge anthu a Israeli...2 Sam 24:4nawerengedwa ngai fumbi...Yes 40:15mphotho siiwerengedwa ya chisomo...Aro4:4[onaninso: yesa]

WERENGA (number)amene adzathe kuziwerenga...Gen 13:16zimene amachita ndi zosawerengeka...Yob 5:9angathe kuwerenga mitambo...Yob 38:37tiphunzitseni kuwerenga masiku...Mas 90:12cha anthu osawerengeka...Chiv 7:9sindingathe kuwerenga zonse...Mas 40:5

Page 160: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

Mulungu wawerenga masiku...Dan 5:26[onaninso: chiwerengero]

WERENGA (read)simudawerenge malembo aja...Mat 21:42naimirira kti awerenge mau...Luk 4:16anthu onse aidziwe ndi kumaiwerenga...2 Akor 3:15kalatayi itawerengedwa pakati...Akol 4:16

WERENGEDWA (accounted)kunawerengedwa...Agal 3:6kudawerengedwa kwa...Yak 2:23[onaninso: yesa]

WERENGERA (account)adzawerengera mlandu...Mat 12:36adzadziwerengera mlandu...Aro 14:12undiwerengere ine...Fil 18monga akuwerengerani...Aheb 13:17[onaninso: lembera]

WERUZA (condemn)kuti akaweruze dziko lapansi...Yoh 3:17wokhulupirira iye saweruzidwa...Yoh 3:18[onaninso: langa, tsutsa]

WERUZA (excutes)pakuweruza molungama...Mas 9:16Yehova amaweruza mwachulungamo...Mas 103:6[onaninso: zenga mlandu]

WERUZIDWA (condemned)wosakhulupirira waweruzidwa...Yoh 3:18[onaninso: tsutsa, tsutsidwa]

WETA (shepherd)akhale oweta ng’ombe...Gen 46:34kuti muwete eklesia wa Mulungu...Mac 20:28wetani gulu la Mulungu...1 Pet 5:2[onaninso: mbusa]

WINA (another)uyang’aniro wake atenge wina...Mac 1:20mukondane wina ndi mnzake...Yoh 13:34[onaninso: yina]

WIRINGULA (excuse)mtima umodzi anayamba kuwiringula...Luk 14:18opanda mau akuwiringula...Aro 1:20kuti tirikuwiringula kwa inu...2 Akor 12:19[onaninso: chowiringula, phophonya]

WOBADWA WOYAMBA (first born)wobadwa woyamba woturuka mwa akufa...Akol 1:18wobadwa woyamba wa akufa...Chiv 1:5[onaninso: ana achisamba, mwana wachisamba]

WOBWERERA M’MBUYO (backslider)wobwerera m’mbuyo m’mtima...Miy 14:14

WOBWEZERA (avenger)kuti muwaletse mdani ndi wobwezera chilango...Mas 8:2wakukwiyira ndi kubwezera chilango ochita choipa...Aro 13:4Ambuye ndiye wobwezera izi zonse...1 Ates 4:6[onaninso: wolipsa]

WOBZYALA (sower)ndi kuipatsitsa mbeu kwa obzyala...Yes 55:10[onaninso: wofesa]

WOCHENJERA (crafty)Jonadabu anali munthu wochenjera...2 Sam 13:3

ziwembu za ochenjera...Yob 5:12atavala zadama wochenjera mtima...Miy 7:10koma pokhala wochenjera ine...2 Akor 12:16[onaninso: mochenjera]

WOCHIMWA (sinner)wochimwa amampatsa ntchito...Mlal 2:28wochimwa amati akachita...Mlal 8:12wochimwa mmodzi amatha...Mlal 9:18onani mkazi wochimwa...Luk 7:37wochimwa amene watembenuka...Luk 15:7munthu wochimwa nkuchita...Yoh 9:16nanga munthu wochimwa...1 Pet 4:18

WODALA (blessed)wodala munthuyo wosayenda...Mas 1:1wodala munthuyu Yehova...Mas 32:2wodalitsidwa mtundu wa anthu...Mas 33:12wodala iye amene asamalira...Mas 41:1wodala wakudzayo m’dzina la...Mas 118:26wodala iye amene awerenga...Chiv 1:3Wodala iye amene adikira...Chiv 16:15Wodala iye amene asunga mau...Chiv 22:7[onaninso: dala, dalitsa, dalitsidwa, dalitsika, odala]

WODALA (happy)wodala munthu amene anadza...Mas 127:5ngodala anthu olandira...Mas 144:15wodala ndi wopeza nzeru...Miy 3:13wokhulupirira Yehova adala...Miy 16:20wodala munthu amene amatsata...Miy 29:18ngodala amene mtima wake...Aro 14:22

WODZICHEPETSA (humble)wosweka ndi wodzichepetsa...Yes 57:15[onaninso: chepetsa, odzichepetsa, ofatsa, ozunzika, wofatsa]

WODZODZEDWAYO (messiah)wodzodzedwayo, ndiye Kalonga...Dan 9:25[onaninso: Mesiya]

WOFATSA (humble)Mose ndiye wofatsa woposa...Num 12:3[onaninso: chepetsa, odzichepetsa, ofatsa, ozunzika,

wodzichepetsa]

WOFESA (sower)wofesa mbeu zabwino...Mat 13:37[onaninso: wobzyala]

WOGULA (buyer)wogula ati...Miy 20:14monga ndi wogula...Yes 24:2wogula asakondwere...Ezek 7:12

WOIPA (evil)wopanduka ndi woipa...Ezara 4:12chomwe woipa...Miy 10:23mutipulumutse kwa woipa...Mat 6:13ndi munthu woipa atulutsa zoipa m’chuma chake choipa...Mat12:35[onaninso: choipa, oipa, zoipa]

WOIPA (wicked)munthu woipa asungika...Yob 21:30woipa sadzakhalaponso...Mas 37:10munthu woipa amazonda...Mas 37:32koma woipa adzagwa...Miy 11:5woipa mtima amangodzithawira...Miy 28:1ndipo woipayo samkhudza...1 Yoh 5:18dziko lapansi ligona mwa woipayo...1 Yoh 5:19[onaninso: oipa, wonyenga, woparamula]

Page 161: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

WOKONDEDWA (beloved)wokondedwa wa Yehova...Deut 33:12wokondedwa wanga...Nyi 1:13wokondedwa wanga ndi wa ine...Nyi 2:16wokondedwa wanga ali...Nyi 5:10wokondedwa kwambiri...Dan 9:23ndiyimbire wokondedwa wanga...Yes 5:1uyu ndiye mwana wanga wokondedwa...Mat 3:17kwa ufulu mwa wokondedwayo...Aef 1:6mbale wokondedwa... File 16uyu ndi mwana wanga wokondedwa...2 Pet 1:17Luka sing’anga wokondedwa...Akol 4:14monganso mbale wathu wokondedwa...2 Pet 3:15ndi mudzi wokondedwawo...Chiv 20:9[onaninso: okondedwa]

WOKONGOLA (borrower)wokongola ndiya kapolo...Miy 22:7[onaninso: wombwereka]

WOKONGOLETSA (creditor)wokongoletsa agwire zonse ali nazo...Mas 109:11munthu wokongoletsa ndalama...Luk 7:41[onaninso: okongoletsa]

WOKONGOZA (lender)ndiye kapolo wa womkongoletsa...Miy 22:7

WOLAMULA (ruler)mfumu yolamulira anthu anga...2 Sam 7:8wolamula akamamvera zamabodza...Miy 28:15amene adzakhala wolamulira...Mika 5:2

WOLAMULIRA (overseer)kapitawo kapena wolamulira...Miy 6:7[onaninso: woyang’anira]

WOLAPA (contrite)apulumutsa iwo a mzimu wolapadi...Mas 34:18mtima wosweka ndi wolapa...Mas 51:17

WOLEMERA (cruel)cha kuwawa mtima ndi ukapolo wolemera...Eks 6:9[onaninso: nkhanza, nkharwe]

WOLENGA (creator)ndikusiya wolengayo...Aro1:25m’manja a wolenga wokhulupirika...1 Petro 4:19[onaninso: mlengi]

WOLENGEDWA (creation)ali wolengedwa mwatsopano...2 Akor 5:17komatu wolengedwa watsopano...Agal 6:15[onaninso: chilengedwe, cholengedwa]

WOLIPSA (avenger)wolipsa mwazi mwini wache aphe wakupha...Num 35:19[onaninso: wobwezera]

WOLONGOLOLA (contentious)kupambana kukhala ndi mkazi wolongolola...Miy 21:19pamodzi ndi mkazi wolongolola...Miy 25:24

WOLOWA NYUMBA (heir)wolowa nyumba ali wakhanda...Agal 4:1wolowa nyumbanso wa Mulungu...Agal 4:7anamuika wolowa nyumba...Aheb 1:2nakhala wolowa nyumba wachilungamo...Aheb 11:7[onaninso: wolowa dzina]

WOLOWA DZINA (heir)

alibe wolowa dzina...Yer 49:1[onaninso: wolowa nyumba]

WOLUNGAMA (righteous)azimasula wolungama namange woipa...Deut 25:1iwe ndiwe wolungama woposa ine...1 Sam 24:17wobadwa ndi mkazi kuti akhale wolungama...Yob 15:14koma wolungama asungitsa njira yake...Yob 17:9woyesa mitima ndi imso ndiye Mulungu wolungama...Mas 7:9akapasuka maziko, wolungama angachitenji...Mas 11:3masautso a wolungama mtima achuluka...Mas 34:17koma wolungama achitira chifundo napereka...Mas 37:17ndipo sindinapenya wolungama wasiyidwa...Mas 37:25wolungama adzakumbukira kunthawi zosatha...Mas 112:6Yehova ali wolungama mnjira zake zonse...Mas 145:17Yehova samvetsa njala moyo wa wolungama...Miy 10:3mkamwa mwa wolungama ndi kasupe wa moyo...Miy 10:11ntchito za wolungama zipatsa moyo...Miy 10:16chiyembekezo cha wolungama ndicho chimwemwe...Miy

10:28wolungama apulumuka kuvuto...Miy 11:8wolungama asamalira moyo wa choweta chake...Miy 12:10wolungama atsogolera mnzake koma njira ya...Miy 12:26mnyumba ya wolungama muli katundu wambiri...Miy 15:6wolungama athamangiramo napulumuka...Miy 18:10wolungama asamalira mlandu wa osauka...Miy 29:7usapambanitse kukhala wolungama...Mlal 7:16kanthu kamodzi kangogwera wolungama ndi woipa...Mlal 9:2nenani za wolungama kuti kudzamkomera iye...Yes 3:10kuti mtundu wolungama umene uchita zoonadi ulowemo...Yes26:2mtumiki wanga wolungama adzalungamitsa ambiri...Yes

53:11wolungama atayika ndipo palibe munthu wosamalirapo...Yes57:1wolungama ndinu Yehova pamene nditsutsana nanumlandu...Yer 12:1popeza agulitsa wolungama ndi ndalama...Amos 2:6zoonadi munthu uyu anali wolungama...Luk 23:47palibe m’modzi wolungama, inde palibe m’modzi...Arom 3:10munthu adzafera wina wolungama...Arom 5:7amene anachitidwa umboni nayo kuti anali wolungama...Aheb11:4ndiye Yesu Khristu wolungama...1 Yoh 2:1wakuchita cholungama ali wolungama...1 Yoh 3:7[onaninso: chilungamo, olungama, zolungama]

WOMANGA (maker)womanga wake ndiye Mulungu...Aheb 11:10[onaninso: mlengi]

WOMBWEREKA (borrower)moteronso ndi wom’bwereka...Yes 24:2[onaninso: wokongola]

WONYENGA (deceitful)mundilanditse kwa munthu wonyenga...Mas 43:1mtima ndiwo wonyenga...Yer 17:9otere ali atumiki onyenga...2 Akor 11:13

WONYENGA (deceiver)wotembereredwa wonyengayo...Malaki 1:14takumbukira kuti wonyenga uja...Mat 27:63pakuti onyenga ambiri adaturuka...2 Yoh 7

WONYENGA (unjust)anatama kapitao wonyengayo...Luk 16:8[onaninso: osalungama, oipa, wosalungama]

WONYENGA (wicked)mtima ndiwo wonyenga...Yer 17:9

Page 162: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: oipa, woipa, woparamula]

WOONONGA (destroyer)ndingalowe m’njira za woononga...Mas 17:4ndi munthu woononga zinthu...Miy 18:9naonongeka ndi woonongayo...1 Akor 10:10

WOOPA MULUNGU (devout)wolungama ndi woopa Mulungu...Luk 2:25[onaninso: okonda Mulungu, opembedza, wopembedza

Mulungu]

WOPANDA MWANA (childless)popeza ndine wopanda mwana...Gen 15:2munditenge ngati wopanda ana...Yer 22:30

WOPARAMULA (wicked)wosamasula ndithu woparamula...Nah 1:3[onaninso: oipa, woipa, wonyenga]

WOPEMBEDZA MAFANO (idolater)wopembedza mafano...1 Akor 5:11oipa ali ngati wopembedza fano...Aef 5:5

WOPEMBEDZA MULUNGU (devout)anali munthu wopembedza Mulungu...Mac 10:7[onaninso: okonda Mulungu, opembedza, woopa Mulungu]

WOPEMBEDZA (religion)adziyesera ali wopembedza...Yak 1:26[onaninso: chipembedzero, kupembedza, mapembedzedwe]

WOPEMBEDZERA ( intercessor)kuti palibe wopembedzera...Yes 59:16

WOPEREKA MALAMULO (lawgiver)Yehova ndiye wotipatsa malamulo...Yes 33:22woika lamaulo ndi woweruza...Yak 4:12

WOPHUNZIRA (disciple)wophunzira saposa mphunzitsi...Mat 10:24chifukwa chakuti ndi wophunzira...Mat 10:42aliyense wofuna kukhala wophunzira...Luk 14:26wophunzira uja amene Yesu amkamukonda...Yoh 21:7[onaninso: ophunzira]

WOPUSA (fool)munthu wopusa amati...Mas 14:1zimeneamachita munthu wopusa...Miy 12:15wopusa amaonetsa poyera uchitsiru...Miy 13:16kwambiri kwa munthu wopusa...Miy 24:7ndasanduka wopusa...2 Akor 12:11[onaninso: chitsiru]

WOPUSA (foolish)ngati mkazi wopusa...Yob 2:10ndinali wopusa wosamvetsa...Mas 73:22koma wopusa amalipasula...Miy 14:1munthu wopusa amachiwononga...Miy 21:20nzeru zapansi pano nkopusa...1 Akor 1:20[onaninso: opusa, zopusa]

WOSAFUFUMITSA (unleavened)buledi wosafufumitsa...Eks 12:17odya buledi wosafufumitsa...Marko 14:1muchotse chofufumitsa...1 Akor 5:7

WOSALAKWA (innocent)konde, ndipo sindidalakwe...Gen 20:5kuonetsa kuti ndine wosalakwa...Mas 73:13usaphe munthu wosalakwa...Eks 23:7

kuti aphe munthu wosalakwa...Deut 27:25kuti azunze munthu wosalakwa...Mas 15:5adaona kuti ndine wosalakwa...Dan 6:22[onaninso: osachimwa]

WOSALANKHULA (dumb)lilime la wosalankhula...Yes 35:6mzimu wosalankhula ndi wogontha...Marko 9:25

WOSALANKHULA (mute)wosamva kapena wosalankhula...Eks 4:11chete osalankhula kanthu...Mas 39:2[onaninso: mbwebwe]

WOSALUNGAMA (unjust)kuti Mulungu ngwosalungama...Aro 3:5pakuti Mulungu sali wosalungama...Aheb 6:10Iye wakukhala wosalungama...Chiv 22:11[onaninso: osalungama, oipa, wonyenga]

WOSAONA MWANA (barren)asungitsa nyumba mkazi wosaona mwana...Mas 113:9[onaninso: chumba, kusabala, opanda zipatso, uma]

WOSAONONGEKA (endless)ya moyo wosaonongeka...Aheb 7:16[onaninso: kosalekeza, wosatha]

WOSATHA (endless)moyo wake umene uli wosatha...Aheb 7:16[onaninso: kosalekeza, wosaonongeka]

WOSATHA (eternal)kuti ndikalandire moyo wosatha...Mat 19:16adzalandira moyo wosatha...Marko 10:30akhale ndi moyo wosatha...Yoh 3:15mupezamo moyo wosatha...Yoh 5:19ndimazipatsa moyo wosatha...Yoh 10:28kuti apereke moyo wosatha...Yoh 17:2moyo wosathawo...Yoh 17:3Mulungu adzawapatsa moyo wosatha...Aroma 2:7moyo wosatha mwa Khristu...Aroma 6:23mpaka ulandira moyo wosatha..1 Tim 6:12chiyembekezo cha moyo wosatha...Tit 1:2ndi a chiweruziro chosatha...Aheb 6:2tikulalikirani za moyo wosatha...1Yoh 1:2wopha anthu, alibe moyo wosatha...1 Yoh 3:15Mulungu adatipatsa moyo wosatha...1 Yoh 5:11mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha...1 Yoh 5:13cha Mulungu podikira moyo wosatha...Yuda 21[onaninso: muyaya]

WOSAUKA (poor)wosauka asadzapereke...Eks 30:15munthu wosaukayu adalira...Mas 34:6amakweza munthu wosauka...Mas 113:7wolemera ndi wosauka akulingana...Miy 22:2wosauka amene amapondereza...Miy 28:3munali munthu wina wosauka...Mlal 9:15anthu amene ali wosauka...Mat 5:3[onaninso: mphawi, osauka]

WOSIYIDWA (desolate)sudzatchedwanso wosiyidwa...Yes 62:4[onaninso: bwinja, ndekhandekha]

WOTSUTSANA (disputer)ali kuti wotsutsana...1 Akor 1:20

WOUKIRA KHRISTU (anti-Christ)mudamva kuti kukubwera woukira Khristu...1 Yoh 2:18ameneyo ndiye woukira Khristu...1 Yoh 2:22

Page 163: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ndi ochokera kwa oukira Khristu...1 Yoh 4:3ndiponso woukira Khristu...2 Yoh 1:7

WOYAMBA (beginning)woyamba wa chilengo cha Mulungu...Chiv 3:14Alefa ndi Omega, woyamba ndi wotsiriza...Chiv 21:6[onaninso: chiyambi]

WOYAMBA (first)woyamba kudzinenera ayang’anika...Miy 18:17atate wako woyamba...Yes 43:27aliyense akufuna kukhala woyamba...Mat 20:27aliyense afuna kukhala woyamba...Marko 10:44munthu woyamba uja...1 Akor 15:45kuti ife amene tinali oyamba...Aef 1:12Ine ndine woyamba ndi wotsiriza...Chiv 1:17[onaninso: yamba]

WOYAMBITSA (author)Yesu amene ali woyambitsa...Aheb 12:2

WOYANG’ANIRA (bishop)ngati munthu akhumba udindo wa woyang’anira mpingo...1Tim 3:1woyang’anira ayenera kukhala...Tit 1:7

WOYANG’ANIRA (overseer)woyang’anira zonse za m’nyumba...Gen 39:4adakuikani wokuyang’anirani...Mac 20:28mbusa amene ali woyang’anira...1 Pet 2:25musaziyang’anire ngati kuti wina...1 Pet 5:2[onaninso: wolamulira]

WOYERA (holiness)wolemekezedwa, woyera, woopsa pomyamika...Eks 15:11[onaninso: chiyeretso, chiyero, patulika]

WOYERA (Holy)woyera, woyera, woyera, Yehova...Yes 6:3pakati mwa Mzimu Woyera...Mat 1:18adzakubatizani ndi Mzimu Woyera...Marko 1:8si ndinu koma Mzimu Woyera...Marko 13:11Mzimu Woyera adzafika pa...Luk 1:35ndipo Mzimu Woyera anatsika...Luk 3:22kumwamba adzapatsa Mzimu Woyera...Luk 11:13Mzimu Woyera adzaphunzitsa...Luk 12:12ankanena za Mzimu Woyera...Yoh 7:39Mzimu Woyera akadzabwera...Mac 1:8adadzazidwa ndi Mzimu Woyera...Mac 2:4Mzimu Woyera waperekedwa...Mac 8:18Mzimu Woyera adawatsikira...Mac 11:15agwirizana ndi a Mzimu Woyera...Mac 15:28kodi mudalandira Mzimu Woyera...Mac 19:2mau amene Mzimu Woyera...1 Akor 2:13pakukupatsani Mzimu Woyera...Aef 1:13nkulandira nao Mzimu Woyera...Aheb 6:4mphamvu ya Mzimu Woyera...1 Pet 1:12adakuitanani ali Woyera...1 Pet 1:15muzikhala oyera mtima...1 Pet 16Mzimu Woyera adawalankhulitsa...2 Pet 1:2mudadzodzedwa ndi Woyera uja...2 Yoh 2:20iye amene ali woyera...Chiv 15:4paja ndi nokha oyera...Chiv 3:7woyera mtima apitirire...Chiv 22:11[onaninso: patulika, yera]

WUNIKIRA (enlighten)mundiwunikire kuti ndingagone...Mas 13:3amandiwunikira mumdima...Mas 18:28kale Mulungu adawawunikira...Aheb 6:4

Y

YAMBA (began)

pomwepo anthu anayamba kutchula...Gen 4:26popeza mudayamba ndi mzimu...Agal 3:3iye amene anayamba mwa inu...Afil 1:6

YAMBA (first)uthenga wabwino uyenera uyambe...Marko 13:10kuyambira mu Yuda…Arom 2:9ndani adayambapo wapereka...Aro11:35paja Adamu ndiye adayambira...1 Tim 2:13pakuti loyamba lija likadakhala...Aheb 8:7anayamba Iye kutikonda...1 Yoh 4:19chikondi choyamba...Chiv 2:4kuuka kwa akufa koyamba...Chiv 20:5[onaninso: woyamba]

YAMBIRI (abundance)popeza kumveka mkokomo wa mvula yambiri...1 Maf 18:41[onaninso: chuluka, chuma, mphamvu, ukulu, sefukira,

zonona]

YAMIKA (bless)potero ndidzakuyamikani m’moyo mwanga...Mas 63:4timayamika Ambuye ndi Atate nalo...Yak 3:9[onaninso: dalitsa, lemekeza]

YANDIKIRA (approach)ndi kumyandikizitsa...Mas 65:4nakondwera kuyandikira...Yes 58:2tsiku lirikuyandikira...Aheb 10:25[onaninso: sendeza]

YANDIKIRA (hand)ufumu wakumwamba wayandikira...Mat 3:2[onaninso: dzanja, manja, mkono, pafupi]

YANDIKIZA (near)kundikomera kuyandikiza kwa...Mas 73:28[onaninso: pafupi]

YANG’ANA (look)munthu adzayang’ana kwa Mlengi...Yes 17:7tayang’ana pa Ziyoni...Yes 33:20tayang’ana kwa Ine...Yes 45:22tiyang’anira kuunika...Yes 59:9tiyang’anira chiweruzo koma...Yes 59:11Israeli sanathe kuyang’anitsa...2 Akor 3:9[onaninso: cheuka, penya]

YANG’ANA (looked)anayang’ana iye nasungunuka...Mas 34:5tinayang’anira mtendere...Yer 8:15anapotoloza, nayang’ana Petro...Luk 22:61[onaninso: penya, penyerera]

YANG’ANA (looking)chikhasu, nayang’ana za...Luk 9:62kuyang’anira kuti pangakhale...Aheb 12:15

YANG’ANA (looks)munthu akuyang’anira kumwamba...Yes 2:11yense wakuyang’ana mkazi...Mat 5:28

YANG’ANA (see)usayang’ane nkhope yake...1 Sam 16:7[onaninso: ona]

YANG’ANA (watch)mudzayang’ana mayendedwe...Yob 14:16muziyang’ana ku mseu... Nah 2:1

YANJANA (acquaint)udziyanjana naye...Yob 22:21

Page 164: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

uziyanjana msanga...Mat 5:25

YANKHA (answer)koma Mulungu adzayankha...Gen 41:16choti muyankhe...2 Sam 24:13ambiri osayankhika...Yob 9:3ndipo ndidzayankha...Yob 13:22pondizonda iye ndimyankha...Yob 31:14iweyo undiyankhe...Yob 40:7ndiitana ine mundiyankhe...Mas 102:2ndiyankheni mwachikhulupiriro...Mas 143:1mayankhidwe ofatsa...Miy 15:1munthu woyankha zoona...Miy 24:26usayankhe chitsiru...Miy 26:4panalibe wina woyankha...Yes 50:2kuyankha kwa Mulungu kulibe...Mik 3:7kaya ndiyankha bwanji...Luk 12:11ndi kanthu kowayankha... 2 Akor 5:12mukadziwe mayankhidwe anu...Akol 4:6

YANKHA (answers)ukayankha usanamve...Miy 18:13

YEHOVA (Lord)Yehova ndiye mphamvu yanga...Eks 15:2Yehova ndiye wankhondo...Eks 15:3Yehova Mulungu wathu...Deut 6:4musamaphera Yehova Mulungu...Deut 17:1akadziwe kuti Yehova Mulungu...1 Maf 8:60ngati Yehova, ndiye Mulungu...1 Maf 18:21inu ndinu Yehova nokhanu...Neh 9:6Yehova wa makamu…Mas 24:10chathu chifuma kwa Yehova...Mas 89:18tiyimbire Yehova mokondwera...Mas 95:1Yehova ndiye Mulungu wamkulu...Mas 95:3Yehova ngwachifundo...Mas 116:5Yehova azinga anthu ake...Mas 125:2Yehova ndiye wolungama...Mas 129:4Yehova ali pafupi ndi onse...Mas 145:18chifukwa chake Yehova adzadikira...Yes 30:18Yehova ndiye chilungamo...Yer 23:6pakuti Yehova wachita...Yow 2:21Yehova Ambuye, ndiye mphamvu...Hab 3:19Yehova adzakhala mfumu...Zek 14:9[onaninso: Ambuye]

YEMBEKEZA (expect)pa nthawi imene simuyembekeza...Luk 12:40

YEMBEKEZA (hope)inu nonse akuyembekeza...Mas 31:24ndinayembekeza mau anu...Mas 119:147Israeli, uyembekezere Yehova...Mas 130:7kuti munthu ayembekeze...Mali 3:26nayembekeza zosayembekezeka...Aro 4:18ngati tiyembekezera chimene...Aro 8:25tiyembekezera Khristu m’moyo uno...1 Akor 15:19[onaninso: chiyembekezo]

YEMBEKEZA (wait)chimene ndikuyembekeza ndicho...Yob 17:13Inde, yembekeza Yehova...Mas 27:14ndiyembekezera Mulungu...Mas 69:3ndidzayembekeza Chauta...Yes 8:17tiyembekeza kuti Mulungu...Agal 5:5amene timuyembekeza...Afil 3:20anthu amene akumuyembekeza...Aheb 9:28[onaninso: dikira]

YEMBEKEZA (waited)pamene ndinkayembekeza...Yob 30:26ndidayembekeza Chauta...Mas 40:1

ankayembekezera nthawi...Luk 2:25ankayembekezera kudza kwa...Luk 23:51[onaninso: dikira]

YEMBEKEZA (waits)kuyembekezera Mulungu...Mas 62:1umayembekeza Chauta...Mas 130:6[onaninso: dikira]

YEMBEKEZERA (waiting)ndiye woyembekezera ufumu wa Mulungu...Luk 23:51[onaninso: dikira, kulindira]

YENDA (move)choyenda kuchokera kuvuma...Zek 14:4timayenda ndipo timakhala...Mac 17:28

YENDA (walk)akadayenda m’njira...Mas 81:13ndimayenda pamaso pa...Mas 116:7ndiyende pakati pa mavuto...Mas 138:7uzisamala mayendedwe ako...Mlal 5:1tiyeni tiyende mkuwala...Yes 2:5njira ndi iyi muyende ...Yes 30:21adzayenda koma osalefuka...Yes 40:31yendani pakati pa zikuni...Yes 50:11olungama amayendamo...Hos 14:9uziyenda mozichepesa...Mik 6:8yako, yamba kuyenda...Yoh 5:8yendani pamene kuwalako...Yoh 12:35mayendedwe athu...Aro 13:13muziyenda ngati anthu...Aef 5:8amayenda motsata chitsanzo...Afil 3:17mudzatha kuyenda m’njira...Akol 1:10m’mene muziyendera kuti...1 Ates 4:1adzayenda nane pamodzi...Chiv 3:4amene nkayenda mumdima...Yes 9:2ankayenda mokhulupirika...Mal 2:6Yesu sankayenda poyera...Yoh 11:54

YENDA (walking)Chauta akuyenda...Gen 3:8anai akungoyenda m’moto...Dan 3:25namayendayendabe m’malamulo...Luk 1:6adaona Yesu akuyenda...Yoh 6:19ankayenda moopa Ambuye...Mac 9:31sukuyendanso m’chikondi...Aro 14:15osayendayenda mochinjera...2 Akor 4:2akuyenda motsata choonadi...2 Yoh 4

YENDA (walks)amayenda pakati pa zithando...Deut 23:14mayendedwe a anthu ochimwa...Mas 1:1munthu amene amayenda...Mas 15:2munthu woyenda mwaungwiro...Miy 10:9woyenda ndi anthu...Miy 13:20amayenda mokhulupirika...Miy 28:18ochimwa sadzayendabe...Yes 35:8woyenda mu mtima...Yes 50:10munthu woyenda molungama...Mik 2:7munthu akayenda masana...Yoh 11:9yendani pamene kuwalako...Yoh 12:35amakhala akuyenda uku...1 Pet 5:8akuyenda mumdima...1 Yoh 2:11

YENERA (appointed)awapulumutse amene anayenera kuphedwa...102:20[onaninso: ika, lembedwa]

YENERA (deserve)muwabwezere zoyenera iwo...Mas 28:4

Page 165: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

YENERA (fitting)kodi kuyenera kunena kwa...Yob 34:18wopusa sayenera kukhala...Miy 19:10ulemu suyenera chitsiru...Miy 26:1kukachita zinthu zosayenera...Aro 1:28wa ansembe wotere anayenera...Aheb 7:26

YENERA (worthy)sindiyenera kulandira chifundo...Gen 32:10ndine wosayenera ngakhale...Mat 3:11oitanidwa aja anali osayenera...Mat 10:11koma oyitanidwawo sanayenera...Mat 22:8ameneyu ngwoyeneradi kuti...Luk 7:4sindiri woyenera kutchedwanso...Luk 15:19nyengo yatsopano sayenera...Aro 8:18sindine woyenera konse...1 Akor 15:9mudziyenda moyenerana... Aef 4:1wantchito ngwoyenera kulandira...1 Tim 5:18pansi pano, sipadawayenere...Aheb 11:38zoyera pakuti ndiwoyeneradi...Chiv 3:4ndinu oyenera kulandira...Chiv 4:11ngwoyenera kulandira...Chiv 5:12

YERA (clean)pakati pa zinthu zoyera...Lev 10:10adzatulutsa choyera mchinthu chodetsa...Yob 14:4woyera m’manja ndi woona mtima...Mas 24:4sambani, dziyeretseni, chotsani...Yes 1:16ndidzakuwazani madzi oyera...Ezek 36:25ndipo adzayeretsa padwale pake...Mat 3:12zonse zili zoyera kwa inu...Luk 11:41koma ayera monse...Yoh 13:10anati, simuli oyera nonse...Yoh 13:11[onaninso: konza]

YERA (holy)tilandireko kuyera mtima...Aheb 12:10koma kuti tikhale oyera...1 Ates 4:7waimapowo ngoyera...Eks 3:5ndiponso ngati mtundu woyera...Eks 19:6Sabata, uzilisunga loyera...Eks 20:8zinthu zoyera ndi zinthu za wamba...Lev 10:10Mulungu wanu, ndine woyera...Lev 19:2palibe woyera wina wofanana...1 Sam 2:2kwa yani wa oyera...Yob 5:1amakhala pampando wake woyera...Mas 47:8pa phiri lake loyera...Mas 48:1kuti tikhale oyera...Aef 1:4[onaninso: patulika, woyera]

YERA (white)ndipo adzakhala oyera...Dan 12:10pamodzi atavala zoyera...Chiv 3:4adzamuvekanso zovala zoyera...Chiv 3:5ndidaona kavalo woyera...Chiv 6:2mikanjo yao ndi kuyeretsa...Chiv 7:14mpando wachifumu woyera...Chiv 20:11

YERETSA (cleanse)ndipo uyeretsa guwa la nsembe...Eks 29:36ndipo mundiyeretse kundichotsera...Mas 51:2mnyamata adzayeretsa mayendedwe...Mas 119:9ndidzakuyeretsani kukuchotserani...Ezek 36:25atamyeretsa ndi kumsambitsa...Aef 5:26udzayeretsa chikumbumtima chanu...Aheb 9:14yeretsani mitima, a mitima iwiri inu...Yak 4:8[onaninso: konza]

YERETSA (cleansed)ndinayeretsa mtima wanga...Mas 73:13munthu adziyeretsa yekha pa izi...2 Tim 2:21[onaninso: yeretsedwa]

YERETSA (hallow)wa makamu, Iye mudzamyeretsa...Yes 8:13iwo adzayeretsa dzina langa...Yes 29:23iwo adzayeretsa woyera wa...Yes 29:23Mulungu Woyera wayeretsedwa...Yes 5:16

YERETSEDWA (cleansed)koma sunayeretsedwa...Ezek 24:13[onaninso: yeretsa]

YESA (accounted)ndipo chinayesedwa kwa iye...Gen 15:6adamuyesa iye...Mas 106:31amene ayesa...Aro 4:5timayesedwa monga...Aro 8:36[onaninso: werengedwa]

YESA (count)sindiuyesa kanthu moyo...Mac 20:24tsono undiyesa woyanjana...Fil 17monga ena achiyesa chizengerezo...2 Pet 3:9chitsiru chikatonthola achiyesa...Miy 17:28anandiyesa wokhulupirika...1 Tim 1:12akuweruza bwino ayesedwa oyera...1 Tim 5:17[onaninso: werenga]

YESA (examine)mundiyesere Yehova...Mas 26:2koma munthu aziyese yekha...1 Akor 11:28koma yense ayesere ntchito yake...Agal 6:4

YESA (exercise)a anthu amadziyesa okha...Luk 22:25[onaninso: chita, chizolowezi cha thupi]

YESA (measured)ndani wayesa madzi...Yes 40:12ndi muyeso umene muyesa...Mat 7:2ndipo anayesa linga...Chiv 21:17

YESA (measuring)anayesa chimangidwecho...Eze 40:5ndi chingwe choyesera...Zek 2:1iye wakuyesa kuti ali...1 Akor 10:12podziyesera okha ndi...2 Akor 10:12

YESA (tempt)chifukwa chiyani mukuyesa...Eks 17:2“usawayese Ambuye … Mat 4:7kuti Satana angakuyeseni...1 Akor 7:5pamene munthu akuyesedwa...Yak 1:13anai, Satana akumuyesa...Marko 1:13sangalole kuti muyesedwe...1 Akor 10:13inu nomwe mungayesedwe...Agal 6:1adazunzidwapo ndi kuyesedwa...Aheb 2:18adayesedwa pa zonse...Aheb 4:15aliyense amayesedwa ndi zinyengo...Yak 1:14kuti tigwe m’zotiyesa...Mat 6:13kuti mungagwe m’zokuyesani...Mat 26:41pa nthawi ya kuyesedwa...Luk 8:13

YESA (test)Mulungu wafika kuti akuyeseni...Eks 20:20ku Yerusalemu kudzamuyesa...1 Maf 10:1amapenya anthu onse ndi kuwayesa...Mas 11:4ndidzawayesa monga m’mene...Zek 13:9kodi mukundiyesa dala...Mat 22:18mudapangana kuyesa Mzimu...Mac 5:9mukumuyeseranji Mulungu...Mac 15:10ndi umene udzayesa...1 Akor 3:13mudziziyesa nokha inuyo...2 Akor 13:5

Page 166: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

zonse muziziyesa bwino...1 Ates 5:21muziwayesa maganizowo...1 Yoh 4:1

YESA (tested)Mulungu adamuyesa Abrahamu...Gen 22:1muyese mtima wanga...Mas 17:3iwo adayesa Mulungu...Mas 78:8ndidakuyesani kumadzi...Mas 81:7anu anandiputa mondiyesa...Mas 95:9adawamvera, nawayesa masiku...Dan 1:14iwonso ayambe ayesedwa...1 Tim 3:10anu adaandiputa pakundiyesa...Aheb 3:9anayesedwa ndi moto...1 Pet 1:7mwayesa ndipo mwawapeza...Chiv 2:2

YESA (tests)amene mumayesa maganizo...Mas 7:9siliva mumayesa...Miy 17:3

YESA (think)chifukwa ayesa kuti adzamvedwa...Mat 6:7kuti asadziyese koposa kumene ayenera...Aro 12:3[onaninso: ganiza]

YESA (thinks)ngati wina ayesa ali kanthu pokhala ali chabe...Agal 6:3ngati wina adziyesera ali wopembedza...Yak 1:26[onaninso: kumbukira, ganiza]

YESA (thought)mumtima mwao ayesa kuti nyumba zao...Mas 49:11[onaninso: ganiza]

YESAYA (Isaiah)mneneri nthawi ya ulamuliro wa Uziya, Yotamu, Ahazi, ndiHezekiya...Yes 1:1anavomera ku maitanidwe a uneneri...Yes 6:1-13ananenera kwa Hezekiya...2 Maf 19,20analemba za mbiri ya Uziya...2 Mbir 26:22analemba za mbiri ya Hezekiya...2 Mbir 32:32analembedwanso ku Chipangano ChatsopanoMat 1:22,23;3:3;8:17;12:17-21;11:26,27;15:12;1Pet 2:22

YESETSA (endeavouring)muziyesetsa kusunga umodzi...Aef 4:3

YINA (another)nkhoswe yina...Yoh 14:16[onaninso: wina]

YOPOSA (excellent)ndiye wamphamvu yoposa...Yob 37:23[onaninso: zopambana, zoposa]

YUFURATE (Euphrates)mtsinje wa m’munda wa Edeni...Gen 2:17malire a dziko la malonjezano...Gen 15:18;1Maf 4:21,24malo a nkhondo...Yer 46:2,6,10angelo anamangidwirapo...Chiv 9:14

YUNISI (Eunice)mai ake a Timoteo...2 Tim 1:5

YUTIKO (Eutychus)anagona nthawi ya chiphunzitso cha Paulo...Mac 20:9anabwezeretsedwa ku moyo...Mac 20:12

Z

ZACHIFUNDO (alms)popereka zachifundo...Luk 11:41mumpatse mphatso zachifundo...Luk 12:33kudzatula zopereka zachifundo...Mac 24:17

ZACHIFUNDO (charitable)kotero kuti mphatso zako zachifundo...Mat 6:4ntchito zabwino ndi zachifundo...Mac 9:36

ZADOKI (Zadok)wansembe wogwira limodzi ntchito ndi Abiyatara;anakhalabe wokhulupirika kwa Davide...2 Sam 15:24-29;20:25anadzudzulidwa ndi Davide...2 Sam 19:11,12sanatsatire Adoniya, anadzoza Solomoni...1 Maf 1:8-45analowa m’malo mwa Abiyatara...1 Maf 2:35

ZAKA (age)ndipo zaka zanga...Mas 39:5[onaninso: kalamba, msinkhu]

ZAKA (years)zaka zanu zili ngati zanu...Yob 10:5zaka chikwi pamodzi...Mas 90:4zaka za moyo wathu...Mas 90:10zaka zanu sizitha...Mas 102:27anali ndi zaka khumi...Luk 2:42zaka zako sizinakwana...Yoh 8:57zaka zanu sizitha...Aheb 1:12pamodzi naye kwa zaka chikwi...Chiv 20:6

ZAKALE (former)chifundo chanu chakale...Mas 89:49kodi bwanji masiku akale...Mlal 7:10amene aneneri akale...Zek 1:4za makhalidwe anga akale...Agal 1:13

ZAKARIYA (Zacharias)bambo ake a Yohane Mbatizi...Luk 1:5-17

ZAKEYO (Zacchaeus)wokhometsa msonkho wolemera yemwe anatembenukira kwaYesu...Luk 19:1-10

ZAKUDYA (foods)nkumawalamula kusala zakudya...1 Tim 4:3

ZAKUMWA (drinks)za thupi zokha ndi zakudya ndi zakumwa...Aheb 9:10[onaninso: imwa]

ZALA (fingers)amalankhula ndi zala zake...Miy 6:13imene zala zao zinaipanga...Yes 2:8

ZALIMUNA (Zalmuna)mfumu ya Midiyani ...Ower 8:4-21

ZAMA (deep)malo ozama a dziko lapansi...Mas 95:4zodabwitsa zake m’madzi ozama...Mas 107:24[onaninso: bi, kulu, kuya]

ZAMA (depths)anamira mozama ngati mwala...Eks 15:5zozama zomwe zinanjenjemera...Mas 77:16anawayendetsa mozama ngati...Mas 106:9atsikira kozama...Mas 107:26pamene panalibe zozama...Miy 8:24[onaninso: kunsi, kuya, zama]

ZAMOTO (fiery)anatumiza njoka zamoto...Num 21:6kudawakhalira lamulo lamoto...Deut 33:2mudzawaika ngati ng’anjo yamoto...Mas 21:9njoka yamoto youluka...Yes 14:29

Page 167: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ng’anjo yotentha yamoto...Dan 3:6ndi mayesedwe amoto...1 Pet 4:12

ZAMOYO (beasts)monga zamoyo zopanda nzeru...Yuda 10[onaninso: nyama, zirombo]

ZAMOYO (creature)ndipo zamoyo zonse...Chiv 16:3[onaninso: cholengedwa, olengedwa]

ZAMOYO (creatures)zamoyo zinai zodzala ndi maso...Chiv 4:6[onaninso: zolengedwa]

ZAMPHAMVU (wonders)m’dzina lanunso zamphamvu...Mat 7:22[onaninso: zodabwitsa, zozizwa, zozizwitsa]

ZANDIRITSA (drunkenness)chipanda chozandiritsa kwa mitundu...Zek 12:2[onaninso: kuledzera]

ZANGA (goods)gawo limodzi la zanga zonse...Luk 19:8[onaninso: chuma, katundu, zinthu]

ZAREFATI (Zarephath)mzinda wa ku Sidon,komwe Eliya anatsitsimutsa mwana wa mkazi wamasiye...1Maf 17:8-24;Luk 4:26

ZATHUPI (carnal)

koma ndili wathupi...Aro 7:14chisamaliro chathupi... Aro 8:7inu simuli athupi kodi...1 Akor 3:3za nkhondo yathu siziri zathupi...2 Akor 10:4

ZATHUPI (carnally)chisamaliro chathupi ndi imfa...Aro 8:6

ZAZIKULU (marvelous)ali kulankhula m’malilime athu zazikulu za Mulungu...Mac

2:11[onaninso: dabwitsa]

ZEBA (Zebah)mfumu ya ku Midiani yomwe inaphedwa ndi Gideone...Ower8:4-28

ZEBEDEO (Zebedee)nsodzi wa ku Galileya, tate wa Yakobo ndi Yohane...Mat

4:21,22

ZEBULONI (Zebulun)mwana wachisanu ndi chimodzi wa Yakobo ndi Leya...Gen30:19,20uneneri okhudza iye...Gen 49:13-- fuko:linawerengedwa...Num 1:30,31;26:27malo anapatsidwa kwa fukoli...Yos 19:10-16anakhala limodzi ndi Gideoni ku nkhondo...Ower 6:34,35ena anamvera zomwe Hezekiya anafuna kubwezeretsa...2

Mbir 30:10-18Yesu anapita kumalo a fukoli...Mat 4:13-16

ZEDEKIYA (Zedekiah)mfumu yomaliza ya Yuda, malume ndi wolowa m’malo mwaYehoiyakini;analamulira moipa, 2 Maf 24:17-19; 2 Mbir 36:10anaukira Nebukadinezara...2 Mbir 36:11-13anakanidwa ndi Yeremiya...Yer 34:1-22anapita kwa Yeremiya kukapempha nzeru...Yer 37;38anagwidwa ndi kutengeredwa ku Babulo...2 Maf 25:1-7;Yer39:1-7

ZEFANIYA (Zephaniah)amene analemba buku la Zefaniya...Zef 1:1- wansembe komanso mnzake wa Yeremiya nthawi yaulamuliro wa Zedekiya...Yer 21:1

ZEKARIYA (Zechariah)mfumu ya Israeli; wolamulira wotsiriza mu mndandanda waufumu wa Yehu; 2 Maf 15:8-12- mneneri ndi wansembe, Ezara 5:1, Zek 1:1,7

ZELOFEHADI (Zelophehad)wafuko la Manase; amene ana ake asanu akazi anateteza ufuluwa akazi...Num 27:1-7

ZENGA MLANDU (excutes)mpaka atazenga mlandu...Mik 7:9[onaninso: weruza]

ZERUBABELE (Zerubbabel)chidzukulu cha Davide...1 Mbir 3:1-19mtsogoleri wa Ayuda omwe anali ku ukapolo...Neh 7:6,7;Hag2:21-23anamanganso kachisi...Ezr 3:1-10;Zek 4:1-14

ZEZE (harp)okhoza kuomba zeze ndi toliro...Gen 4:21ndi chisakasa ndi zeze...Mas 150:3zonse zili nao azeze...Chiv 5:8

ZIBA (Ziba)wantchito wa Saulo...2 Sam 9:9anachita ubale ndi Davide...2 Sam 16:1-4anadzudzulidwa kuti anali wabodza ndi kunama ndiMefiboseti...2 Sam 19:17-30

ZIBUMA (clodes)zibuma za kuchigwa...Yob 21:33

ZIDA ZA NKHONDO (armor)zida zake anazisunga...1 Sam 17:54tulani nthungo zanu ...Yer. 46:4tivale chamuna cha ...Aro 13:12tavalani zida zonse za ...Aef 6:11

ZIDA ZA NKHONDO (weapons)kupambana zida zankhondo...Mlal 9:18Yehova wanyamula zida...Yes 13:5zida zankhondo si za anthu...2 Akor 10:4

ZIDA (instruments)amagwiritsa ntchito zida...Gen 49:5

ZIDZUKULU (offspring)madalitso anga pa zidzukulu...Yes 44:3[onaninso: ana]

ZIGOLOLO (adulteries)ndi zigololo zako...Yer 13:27ndi zigololo zake...Hos 2:2zigololo...Marko 7:22

ZIKA MIZU (rooted)muzike mizu yanu...Aef 3:17mukhale ozika mizu mwa...Akol 2:7

ZIKHUMBITSO (pleasure)kodi sizichokera ku zikhumbitso zanu...Yak 4:1

Page 168: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: komera, konda, kondwera]

ZIKILAGI (Ziklag)mzinda m’malire a Yuda...Yos 15:1,31anatengedwa ndi Davide...1 Sam 27:6unagonjetsedwa ndi Aamaleki...1 Sam 30:1-31

ZIKONDWERERO (feasts)zikondwerero zanu ndidzazisandutsa...Amo 8:10[onaninso: mapwando]

ZIKOPE (eyelids)ana a anthu ndi zikope zake...Mas 11:4zikope zako zipenya moongoka...Miy 4:25

ZILAKOLAKO (desires)tinkatsata zilakolako za khalidwe...Aef 2:3zimachokera ku zilakolako zanu...Yak 4:1[onaninso: funa, khumba]

ZILALA (cold)cha anthu aunyinji chizazilala...Mat 24:12[onaninso: chisanu, zizira]

ZILIPA (Zilpha)wantchito wamkazi wa Leya...Gen 29:24mai ake a Gadi ndi Asha...Gen 30:9-13

ZILONDA (boils)namzuza Yobu ndi zilonda zowawa...Yob 2:7

ZILONDA (sores) mikwingwirima ndi zilonda...Yes 1:6 iyeyo anali ndi zilonda...Luk 16:20

ZIMIDWA (extinguished)zimidwa ngati lawi…Yes 43:17[onaninso: fafanizika]

ZIMIRI (Zimri)kalonga wa fuko la Simeoni amene anaphedwa ndi Finehasi...Num 25:6-14-mfumu ya Israeli yomwe inangokhala mfumu masiku asanundi awiri...1 Maf 16:8-20

ZINDIKIRA (acknowledge)sanazindikire abale...Deut 33:9ndazindikira machimo...Mas 51:3Israeli satizindikira ...Yes 63:16azindikire kuti ...1 Akor 14:37[onaninso: dziwa, vomera, vomereza]

ZINDIKIRA (comprehend)ndi mdimawu sunakuzindikira...Yoh 1:5mukakhozetu kuzindikira pamodzi...Aef 3:18[onaninso: kumvetsa]

ZINDIKIRA (discern)kodi ndikhonza kuzindikiranso...2 Sam 19:35ndi kuzindikira pakati pa olungama...Mal 3:18mudziwa kuzindikira za pa nkhope...Mat 16:3anazoloweretsa zizindikiritso zao...Aheb 5:14ndipo sakhoza kuzindikira...1 Akor 2:14

ZINDIKIRA (discerner)nazindikiritsa zolingilira...Aheb 4:12

ZINDIKIRA (perceive)mtima wakuzindikira zimenezi...Deut 29:4kapena m’mbuyo sindimzindikira...Yob 23:8imvani inu ndinu, koma osazindikira...Yes 6:9apenye, koma asazindikire...Marko 4:12

ZINDIKIRA (understand)ndiyo yakuti azindikire njira yake...Miy 14:8ndithu koma osazindikira...Yes 6:9unaika mtima wako kuzindikira...Dan 10:12mmodzi wa oipa adzazindikira...Dan 12:10anthu osazindikirawo adzagwetsedwa...Hos 4:14wanzeru ndani kuti azindikire izi...Hos 14:9simuzindikira malankhulidwe...Yoh 8:43nangazindikire ndi mtima...Mac 28:27muli zina zovuta kuzizindikira...2 Pet 3:16[onaninso: dziwa, dziwitsa, mvera, mvetsetsa, nzeru]

ZINDIKIRIKA (understood)popeza zandikirika ndi zinthu zolengedwa...Aro 1:20[onaninso: lingalira, mvetsa, phunzira,]

ZINGA (hedged)amene Mulungu wamzinga...Yob 3:23mumandizinga kumbuyo ndi kutsogolo...Mas 139:5

ZINGA (surround)anazingidwa ndi chikondi...Mas 32:10za imfa zidandizinga...2 Sam 22:5ya imfa idandizinga...Mas 116:3mitundu yonse idandizinga...Mas 118:10zolakwa zao zawazinga...Hos 7:2[onaninso: zinga]

ZINGWE (cords)anadulatu zingwe za oipa...Mas 129:4adzamangidwa ndi zingwe...Miy 5:22akoka mphulupulu ndi zingwe...Yes 5:18ndinawakoka ndi zingwe...Hos 11:4adapanga nkwapulo wa zingwe...Yoh 2:15

ZINI (Zin)chipululu chimene Aisraeli anachidutsa...Num 20:1malire pakati pa Yuda ndi Edomu...Yos 15:1-3

ZINSINSI (mysteries)kudziwa zinsinsi za ufumu...Mat 13:11ndingadziwe zinsinsi zonse...1 Akor 13:2mumzimu alankhula zinsinsi...1 Akor 14:2

ZINSINSI (secrets)adaakululira zinsinsi...Yob 11:6iye amadziwa zinsinsi zonse...Mas 44:21amaulula zinsinsi...Miy 11:13amene amaulula zinsinsi...Dan 2:28adzaweruza zinsinsi...Aro 2:16

ZINTHU (goods)woyang’anira zinthu zake zonse...Mat 24:47[onaninso: chuma, katundu, zanga]

ZINYATSI (filth)tasanduka onyozeka, ngati zinyatsi...1 Akor 4:13[onaninso: litsiro, zonyansa]

ZIPATA (gates)ndi zipata zake zatenthedwa...Neh 1:3mitu yanu zipata inu...Mas 24:7Yehova akonda zipata Ziyoni...Mas 87:2nditsegulireni zipata za chilungamo...Mas 118:19pitani, pitani pa zipata...Yes 62mukhale nazo zipata khumi ndi...Chiv 21:12pa zipata zake sipatsekedwa...Chiv 21:25

ZIPATSO ZAGOLIDI (apples)akunga zipatso zagolidi...Miy 25:11[onaninso: maapulosi]

Page 169: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ZIPATSO (fruits)onetsani inu zipatso zakuyenera...Mat 3:8mudzawazindikira ndi zipatso zao...Mat 7:16nadzaonjezapo pa zipatso zao...2 Akor 9:10zipatso zoundukura za zolengedwa...Yak 1:18yodzala chifundo ndi zipatso zabwino...Yak 3:17ndi kupatsa zipatso zake mwezi ndi...Chiv 22:2

ZIPATSO (fruit)nawaonetsa zipatso za dzikoli...Num 13:26zidzakhala zodala zipatso za...Deut 28:4ndi zipatso za mkamwa mwake...Miy 12:14zipatso zake zinatsekemera...Nyi 2:3adzadya zipatso za machitidwe ao...Yes 3:10zipatso zako zipezeka zochokera...Hos 14:8mtengo ulionse osabala zipatso...Mat 3:10mtengo wabwino ulionse upatsa zipatso...Mat 7:17sakhwimitsa zipatso zamphumphu...Luk 8:14[onaninso: chipatso]

ZIPHUPHU (bribe)olandira ziphuphu moto udapsereza...Yob 15:34dzanja lawo lamanja lodzaza ndi ziphuphu...Mas 26:10munthu wodana ndi ziphuphu...Miy 15:27kuti aipatse ziphuphu...Miy 29:4mulandira ziphuphu...Amo 5:12[onaninso:chiphuphu]

ZIPORA (Zipporah)mwana wamkazi wa Yetero; mkazi wa Mose...Eks 18:1,2

ZIPUTU (straw)mtengo, maudzu, ziputu...1 Akor 3:12[onaninso: phesi]

ZIRIPO (exist)ndi kuitana zinthu zoti palibe, monga ngati ziripo...Aro 4:17[onaninso: khala]

ZIROMBO (beasts)pamenepo zirombo zinalowa...Yob 37:8ngati ndinalimbana ndi zirombo...1 Akor 15:32[onaninso: nyama, zamoyo]

ZISANU (five)zikwi zisanu amuna okha...Mat 14:21[onaninso: asanu, isanu]

ZISONI (sorrowful)masiku ake onse ndi zisoni...Mlal 2:23[onaninso: chisoni, wachisoni, zowawa]

ZISONI (sorrows)zidzachuluka zisoni zao...Mas 16:4munthu wazisoni...Yes 53:3

ZITHUMWA (charms)akazi amene amasoka zithumwa...Ezek 13:18

ZITSANZO (examples)okhala zitsanzo za gululo...1 Pet 5:3

ZITSEKO (doors)tsekulani zitseko zakalekalezo...Mas 24:7atsekeretu zitseko za nyumba yanga...Malak 1:10[onaninso: makomo]

ZITSIME (wells)pokatunga madzi m’zitsime...Yes 12:3

ZITSIRU (fools)

zitsiru ndiye zimanyoza ...Miy 1:7koma zitsiru zimanyengedwa...Miy 14:8zitsiru sizilabadako za kulapa...Miy 14:9Mulungu sakondwera nazo zitsiru...Mlal 5:4

ZIVOMEZI (earthquakes)kudzachitika zivomezi...Marko 13:8

ZIWALA (grasshoppers)amaona anthu pansi ngati ziwala...Yes 40:22akuluakulu anu ali ngati ziwala...Nah 3:17

ZIWALO (members)chimodzi cha ziwalo zako chionongeke...Mat 5:29ziwalo zanu zonse kwa Mulungu...Aro 6:13matupi anu ndi ziwalo za...1 Akor 6:15ndife ziwalo za thupi la Khristu...Aef 4:25

ZIWANDA (demons)anaziphera nsembe ziwanda...Deut 32:17nsembe ya kwa ziwanda...Mas 106:37mphamvu ndi ulamuliro pa ziwanda...Luk 9:1ziwanda zinagonjera ife...Luk 10:17ndi chikho cha ziwanda...1 Akor 10:21ziwanda zikhulupiriranso...Yak 2:19nusandulika mokhalamo ziwanda...Chiv 18:2

ZIYONI (Zion)malo ena ku Yerusalemu; otchedwa mzinda wa Davide...2Sam 5:6-9; 2 Mbir 5:2anagwiritsidwa mwa tanthauzo mu ufumu wa Mulungu...Mas125:1,Aheb 12:22;Chiv 14:1

ZIZIRA (cold)ndani angathe kupirira kuzizira...Mas 147:17ali ngati madzi ozizira...Miy 25:13uli ngati madzi ozizira...Miy 25:25chikho cha madzi ozizira...Mat 10:42sindinu ozizira...Chiv 3:15[onaninso: chisanu, zilala]

ZIZIRITSA (cool)naziziritse lilime langa...Luk 16:24

ZIZWA (astonished)monga ambiri anazizwa...Yes 52:14makamu a anthu anazizwa...Mat 7:28[onaninso: dabwa]

ZIZWA (marveled)pakumva ichi, Yesu anazizwa...Mat 8:10apo anthu onse adazizwa...Mat 9:33[onaninso: dabwa]

ZOBUULA (groanings)ndi zobuula zosatheka kuneneka...Aro 8:26

ZOCHIMWA (faults)ndizakumbukira zochimwa...Gen 41:9[onaninso: zolakwa]

ZOCHULUKA (plentiful)zinthu zochulukadi...Mat 9:37

ZODABWITSA (marvelous)adachita zodabwitsa...Mas 78:12zimenezi nzodabwitsa pamaso...Mas 118:23ntchito zanu zonse nzodabwitsa...Mas 139:14mkuwala kwa kodabwitsa...1 Pet 2:9

ZODABWITSA (strange)nanena kuti taona zodabwitsa...Luk 5:26

Page 170: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: chilendo]

ZODABWITSA (wonders)mumachita zodabwitsa...Mas 77:14zodabwitsa zanu zimadziwika...Mas 88:12amachita zodabwitsa zazikulu...Mas 136:4zodabwitsa zake nzamphamvu...Dan 4:3amachita zizindikiro ndi zodabwitsa...Dan 6:27ndidzaonetsa zodabwitsa izi...Yow 2:30[onaninso: zamphamvu, zozizwa, zozizwitsa]

ZODETSA (filthiness)kukuchotserani zodetsa zanu...Ezek. 36:25kuletsa chodetsa chonse...2 Akor. 7:1ndi chovala chodetsa...Yak 2:2

ZOFARI (Zophar)mnzake wa Yobu wa ku Naama...Yob 2:11

ZOIPA (evil)ndi mtengo wakudziwitsa zabwino ndi zoipa...Gen 2:9wakudziwitsa zabwino ndi zoipa...Gen 3:5amphulupulu adzadzazidwa ndi zoipa...Miy 12:21wobwezera zabwino zoipa...Miy 17:13zoipa sizizamchokera kwao...Miy 17:13mkaziyo amchitira zabwino, si zoipa...Miy 31:12amene ayesa zoipa zabwino ndi zabwino zoipa...Yes 5:20nchifukwa chanji mulikuganizira zoipa m’mitimamwanu...Mat 9:4ndi munthu woipa atulutsa zoipa m’chuma chake choipa...Mat

12:35pakuti yense wakuchita zoipa adana nako kuunika...Yoh 3:20koma ozungulidwa pa zoipa...Aro 16:19sichipsa mtima, sichilingilira zoipa...1 Akor 13:5[onaninso: choipa, oipa, woipa]

ZOIPA (iniquities)zoipa zosawerengeka zandizinga...Mas 40:12anachita zoipa ziwiri...Yer 2:13

ZOIPA (wickedness)wodziwitsa zabwino ndi zoipa...Gen 2:9mudzadziwa zabwino ndi zoipa...Gen 3:5ntchito zake nzoipa...1 Sam 24:13kuipa kwao nkwakukulu...Yob 22:5simufuna zoipa pamaso panu...Mas 5:4thetsani ntchito zoipa... Mas 7:9sapewa zoipa...Mas 36:4umakonda zoipa kupambana...Mas 52:3zoipa zili tho m’mitima...Mas 55:15kuchita zoipa ndiye chakudya...Miy 4:17kulankhula zoipa nchinthu...Miy 8:7adzadzadzidwa ndi zoipa...Miy 12:21wobwezera zabwino zoipa...Miy 17:13zoipa sizizamchokera...Miy 17:13zabwino, si zoipa...Miy 31:12anthu ochita zoipa...Mlal 8:7amene ayesa zoipa...Yes 5:20umasungira zoipa zake…Yer 6:7odzikuza ndi ochita zoipa...Mal 4:1mukuganiza zoipa mumtima...Mat 9:4anatulutsa zoipa mchuma...Mat 12:35aliyense wochita zoipa...Yoh 3:20ndimachita zoipa zimene sindifuna...Aro 7:21muzidana ndi zoipa...Aro 12:9musagonjere zoipazo...Aro 12:21sichilingilira zoipa...1 Akor 12:5za inu ngati ochita zoipa...1 Pet 2:12[onaninso: choipa, ipa]

ZOKHOTA (crooked)kutsata njira zao zokhotakhota...Mas 125:5zokhota zidzaongoledwa...Yes 40:4zokhota zidzakhala zolungama...Luk 3:5mbadwo wokhotakhota...Afil 2:15

ZOKHUMUDWITSA (offenses)chifukwa cha zokhumudwitsa...Mat 18:7[onaninso: zolakwa, zolakwitsa]

ZOKONDWERETSA (pleasures)muli zokondweretsa zonka muyaya...Mas 16:11[onaninso: kondwera]

ZOLAKWA (faults)angathe kudziwa zolakwa...Mas 19:12[onaninso: zochimwa]

ZOLAKWA (offenses)chifukwa cha zolakwa zathu...Aro 4:25[onaninso: zokhumudwitsa, zolakwitsa]

ZOLAKWITSA (offenses)kuti zolakwitsa zisadze...Luk 17:1[onaninso: zokhumudwitsa, zolakwa]

ZOLENGEDWA (creatures)zolengedwa zina zonse zokhala m’madzi...Gen 1:21zoundukula za zolengedwa zake...Yak 1:18[onaninso: zamoyo]

ZOLINGALIRA (thoughts)zolingalira zanu nzozama ndithu...Mas 92:5Yehova adziwa zolingalira za munthu...Mas 94:11ndipo zolingalira zako zidzakhazikika...Miy 16:3[onaninso: maganizo, malingiriro, zolingirira]

ZOLINGIRIRA (thoughts)nazindikira zolingirira zonse za...1 Mbir 28:9ndipo zolingirira zani za pa ife...Mas 40:5koma sadziwa zolingirira za Yehova...Mika 4:14Ambuye azindikira zolingirira za anzeru...1 Akor 3:20[onaninso: maganizo, malingaliro, zolingalira]

ZOLOWEZA (exercise)uzizoloweze kukhala ndi...1 Tim 4:7iwowa adadzizoloweza...Aheb 5:14

ZOLUNGAMA (righteous)pakuti bafuta ndiye zolungama za oyera mtima...Chiv 19:8[onaninso: olungama, wolungama]

ZOMANGIRA (chains)kumbukirani zomangira zanga...Akol 4:18[onaninso: maunyolo, ndende, nkhata, nsinga]

ZOMLEMEKEZA (Psalm)Myimbireni Yehova zomlemekeza...Mas 98:5[onaninso: salimo]

ZONDA (spies)ndinu anthu ozonda...Gen 42:9anyamata ozondawo...Yos 6:23adatuma anthu omuzonda...Luk 20:20

ZONONA (abundance)moyo wanu nukondwere ndi zonona...Yes 55:2[onaninso: chuluka, chuma, mphamvu, ukulu, sefukira,

yambiri]

ZONONA (abundantly)adzakhuta kwambiri ndi zonona za m’nyumba...Mas 36:8

Page 171: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

[onaninso: chuluka, posa]

ZONONA (fatness)ngati ndi mafuta ndi zonona...Mas 63:5

ZONYANSA (filth)ndi kuchotsa zonyansa...Yes. 4:4anali kuvula nsalu zonyansa...Zek 3:3[onaninso: litsiro, zinyatsi]

ZONYANSA (filthy)dumbo, mwano, zonyansa...Akol 3:8ndi mayendedwe onyansa ...2 Pet 2:7ndi munthu wonyansa akhalebe...Chiv 22:11

ZOONA (truth)onani inu mukondwera ndi zoonadi...Mas 51:6chilamulo cha zoona chinali mkamwa mwake...Malak 2:6mudzadziwa zoona zeni zeni...Yoh 8:32Mzimu wodziwitsa zoona...Yoh 16:13ndikunenazi nzoona...Mac 26:25kumalepheretsa kudziwa zoona...Aro 1:18pakulankhula zoona...Aef 4:15ndinena zoona...1 Tim 2:7[onaninso: choona, choonadi, kuona, lungama]

ZOOPETSA (terrors)zoopetsa zidzamchititsa mantha...Yob 18:11[onaninso: zoopsa]

ZOOPSA (terrors)zoopsa za Mulungu zindindandira...Yob 6:4kumka naye kwa mfumu ya zoopsa...Yob 18:14zoopsa zimgwera ngati madzi...Yob 27:20athedwa konse ndi zoopsa...Mas 73:19[onaninso: zoopetsa]

ZOPAMBANA (excellent)nzeru zake nzopambana...Yes 28:29[onaninso: yoposa, zoposa]

ZOPANDA ULEMU (dishonour)koma zina zopanda ulemu...1 Tim 2:20[onaninso: manyazi, mnyozo, peputsa]

ZOPEMPHA (petitions)zonse zimene wapempha...Mas 20:5tilandiradi zimene tapempha...1 Yoh 5:15

ZOPEREKA (collection)kunena za zopereka ...1 Akor 16:1

ZOPEREKA (gifts)ali kuika zopereka zao mosunguramo...Luk 21:1[onaninso: mphatso]

ZOPEREKA (offering)kwa Yehova zopereka m’chilungamo...Mal 3:3[onaninso: chopereka, nsembe]

ZOPEREKA (offerings)likumbukire zopereka zako zonse...Mas 20:3[onaninso: nsembe]

ZOPOSA (excellent)pakuti ndikanena zoposa...Miy 8:6nuvomereza zinthu zoposa...Aro 2:18[onaninso: yoposa, zopambana]

ZOPULULUTSA (desolation)Yehova amene achita zopululutsa...Mas 46:8[onaninso: chipululutso]

ZOPUSA (folly)asabwererenso kuchita zoipa...Mas 85:8[onaninso: uchitsiru]

ZOPUSA (foolish)upewe kufufuzafufuza zopusa...Tit 3:9[onaninso: opusa, wopusa]

ZOPUSA (foolishness)pakuti wopusa adzanena zopusa...Yes 32:6[onaninso: chibwana, kupusa, opusa]

ZOSAONEKA (invisible)makhalidwe osaoneka a Mulungu...Aro 1:20chenicheni cha Mulungu osaoneka...Akol 1:15yamuyaya, yosafa, yosaoneka...1 Tim 1:17woona Mulungu wosaonekayu...Aheb 11:27

ZOSAWERENGEKA (innumerable)yosawerengeka ngati mchenga...Aheb 11:12m’mene muli angelo osawerengeka...Aheb 12:22

ZOTICHENJEZA (admonitions)monga zotichenjeza...1 Akor 10:11

ZOTSUTSANA (contradictions)zopanda pake ndi zotsutsana...1 Tim 6:20

ZOVALA (clothes)zovala zanga zidzanyansidwa...Yob 9:31zovala zake zinakhala zonyezimira...Marko 9:3anayalika zovala zawo pa mwana wa bulu...Luk 19:36zinaika zovala zao pamapazi...Mac 7:58ndi kutaya zovala zao...Mac 22:23ndi chovala chokometsetsa...Yak 2:2

ZOVALA (robes)unawazidwa pa zovala zanga...Yes 63:3ndidzakuveka zovala za mtengo wake...Zek 3:4atavala zovala zoyera...Chiv 7:9[onaninso: miinjiro]

ZOVALA (garments)zovala zanu sizinatha pathupi panu...Deut 8:4umo zovala zanu zifundira...Yob 37:17agawana zovala zanga...Mas 22:18zovala zake nza madeya...Mas 45:13zovala zako zikhale zoyera...Mlal 9:8ndi zovala zovimvinika m’mwazi...Yes 9:5ndi zovala zonika zochokera ku...Yes 63:1ndizakuveka zovala zamtengo wake...Zek 3:4adza kwa inu ndi zovala...Mat 7:15anayala zovala zao panjira...Mat 21:8anagawana zovala zake...Mat 27:35anagawana zovala zanga...Yoh 19:24zovala zanu zajiwa ndi...Yak 5:2motero zovala zoyera...Chiv 3:5[onaninso: chovala]

ZOVUTA (perilous)kudzafika nthawi ya zovuta...2 Tim 3:1

ZOWARI (Zoar)mzinda wakale wa Kanani womwe dzina lake loyamba linaliBela...Gen 14:2,8sunawonongedwe chifukwa cha pempho la Mose...Gen19:20-23

ZOWAWA (grief)ndi wodziwa zowawa...Yes 53:3[onaninso: chisoni]

Page 172: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed

ZOWAWA (hardship)mudziwa zowawa zonse...Num 20:14zowawa pamodzi nane...2 Tim 2:3

ZOWAWA (pained)mtima wanga ukuwawa...Yer 4:19Mulungu adammasula ku zowawa...Mac 2:24zowawa zimachitikira mkazi...1 Ates 5:3[onaninso: ululu]

ZOWAWA (pains)pathupi, udzamva zowawa...Gen 3:16adzavutika ndi kumva zowawa...Yes 13:8asanayambe kumva zowawa...Yes 66:7kulira, kapena kumva zowawa...Chiv 21:4[onaninso: ululu]

ZOWAWA (pangs)ndipo azamva zowawa...Yes 13:8ndi kugwidwa m’zowawa...Aro 8:22[onaninso: nthambo]

ZOWAWA (sorrowful)wozunzika ndi womva zowawa...Mas 69:29[onaninso: chisoni, wachisoni, zisoni]

ZOWETA (cattle)osachepsanso zoweta zao...Mas 107:38[onaninso: ng’ombe]

ZOWETA (flock)adzadyetsa zoweta zake ngati...Yes 40:11dyetsani zoweta zanga...Zek 11:4[onaninso: gulu, gulu la nkhonsa, nkhosa]

ZOZIZWA (wonders)ndi zozizwa zozama...2 Ates 2:9[onaninso: zamphamvu, zodabwitsa, zozizwitsa]

ZOZIZWITSA (miracles)Mulungu adachita zozizwitsa zambiri...Mac 19:11mphamvu zochitira zozizwitsa...1 Akor 12:10mphamvu zakuchita zozizwitsa...1 Akor 12:29zinthu zozizwitsa ndi ntchito...Aheb 2:4

ZOZIZWITSA (wonders)zozizwitsa zomwe ndidzachita...Eks 3:20pochita zizindikiro zozizwitsa...Yer 32:21ndi zozizwitsa ndi mphamvu...Aheb 2:4[onaninso: zamphamvu, zodabwitsa, zozizwa]

ZUNGULIRA (surround)mudzazungulire mfumuyo...2 Maf 11:8

za imfa zidandizungulira...Mas 18:4mweza wam’nyanjamo undizungulira...Yon 2:3pozungulira pali mboni...Aheb 12:1[onaninso: zinga]

ZUNZA (afflict)ndidzazunza zidzukuru...1 Maf 11:39nazunza cholandira chanu...Mas 94:5ndidzachita nawo onse akuzunza iwe...Zef 3:19ndisazunzidwe ndina...Mas 119:67nu mumazunza anthu...Amo 5:12[onaninso: sautsa, vutitsa, zunzika]

ZUNZA (persecute)kodi simunandizunze...Yob 19:22anthuwo amandizunza ndi maboza...Mas 119:86akamakunyozani, kukuzunzani...Mat 5:11awadalitse amene amakuzunzani...Aro 12:14

ZUNZA (persecuted)koma adazunza osauka...Mas 109:16anthu ankazunzira aneneri...Mat 5:12pakuti ndinkazunza mpingo...1 Akor 15:9adani akutizunza...2 Akor 4:9munthu uja ankatizunza kaleyu...Agal 1:23

ZUNZA (persecution)kumzunza ndi kumunyoza...1 Tim 1:13[onaninso: zunzidwa]

ZUNZA (torment)mudzakhala mundizunzabe...Yob 19:2kuno kudzatizunza...Mat 8:29pakuti ndikuzunzika...Luk 16:24adzazunzidwa usana ndi usiku...Chiv 20:10[onaninso: chisoni]

ZUNZA (tormented)ankazunzika kumalo...Luk 16:23mundizunze ndi kundinyoza...Yob 10:3musamazunze akazi amasiye...Zek 7:10ndani amene ndidamuzunza...1 Sam 12:3ndidaonanso kuzunza...Mlal 4:1adamsautsa ndi kumzunza...Yes 53:7

ZUNZA (torments)anthu anga akuzunzikira...Eks 3:7chifukwa cha mazunzo...Mas 107:39kwa anthu ondizunza...Mas 119:134ozunzawo anali ndi...Mlal 4:1kunzunza ena kumasandutsa...Mlal 7:7kulira kwa anthu ozunzidwa...Yes 5:7wa anthu okuzunza...Yes 51:13

ZUNZIDWA (persecution)udayamba kuzunzidwa kwambiri...Mac 8:1nanga bwanji ndikuzunzidwabe...Agal 5:11[onaninso: zunza]

ZUNZIDWA (suffer)chokhacho chakuti angazunzidwe...Agal 6:12

[onaninso: kumva zowawa, phwetekwa]

ZUNZIKA (afflict)adzanenera wozunzika...Mas 140:12munthu wozunzika...Miy 15:15anthu ozunzika ...Yes 58:10[onaninso: sautsa, vutitsa, zunza]

ZUNZIKA (afflicted)ndisanazunzidwe ndinasokera...Mas 119:67

ndazunzika kwambiri...Mas 119:107adzanenera wozunzika mlandu...Mas 140:12[onaninso: sautsa,sautsidwa, osauka]

Page 173: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed
Page 174: CHICHEWA BIBLE CONCORDANCE CONTRIBUTORS: Funded by: Bob and Kathy Brack Translated to Chichewa by: Lombola Gama Junior Edited by: Wesley Albert Kanchepera and Snoya Liwonde Typed